Aionian Verses
Ngakhale kuti ana ake onse aamuna ndi aakazi anasonkhana kudzamutonthoza, iye anakana kutonthozedwa. Iye anati, “Ayi. Ndidzalira mpaka ndidzapite kwa mwana wanga ku manda.” Choncho Israeli anapitirirabe kulira mwana wake. (Sheol )
(parallel missing)
Koma Yakobo anati, “Mwana wanga sapita nanu kumeneko; mkulu wake anamwalira ndipo watsala yekha. Ngati choyipa chitamuchitikira pa ulendo mukupitawu, ndiye kuti ndi mmene ndakalambiramu inu mudzandipha ndi chisoni chotere.” (Sheol )
(parallel missing)
Tsopano mukanditengeranso uyu, nakaphedwa mu njira ndiye kuti mudzandikankhira ku manda ndi chisoni.’ (Sheol )
(parallel missing)
ndipo akakaona kuti mnyamatayu palibe, basi akafa. Ife tidzakhala ngati takankhira abambo athu ku manda ndi chisoni. (Sheol )
(parallel missing)
Koma Yehova akachita china chake chachilendo, nthaka nitsekula pakamwa pake ndi kuwameza iwo pamodzi ndi zonse zimene ali nazo, iwowa nʼkulowa mʼmanda ali moyo, pamenepo mudzazindikira kuti anthu amenewa ananyoza Yehova.” (Sheol )
(parallel missing)
Analowa mʼmanda amoyo pamodzi ndi zonse zimene anali nazo. Nthaka inawatsekera ndi kuwawononga ndipo sanaonekenso. (Sheol )
(parallel missing)
Pakuti mkwiyo wanga wayaka ngati moto, umene umayaka mpaka ku dziko la anthu akufa. Motowo udzanyeketsa dziko lapansi ndi zokolola zake ndipo udzapsereza maziko a mapiri. (Sheol )
(parallel missing)
“Yehova amabweretsa imfa ndipo amaperekanso moyo, amatsitsira ku manda ndipo amawatulutsakonso. (Sheol )
(parallel missing)
Anandimanga ndi zingwe za ku manda; misampha ya imfa inalimbana nane. (Sheol )
(parallel missing)
Iwe uchite kwa iye molingana ndi nzeru zako, koma usalole kuti afe ndi ukalamba ndi kupita ku manda mwamtendere. (Sheol )
(parallel missing)
Koma tsopano usamuyese ngati munthu wosalakwa. Iwe ndiwe munthu wanzeru. Udzadziwa choti uchite naye. Ngakhale ndi wokalamba, aphedwe ndithu.” (Sheol )
(parallel missing)
Monga mtambo umazimirira ndi kukanganuka, momwemonso munthu amene walowa mʼmanda sabwerera. (Sheol )
(parallel missing)
Zili kutali kupambana mayiko akumwamba, nanga ungachite chiyani? Ndi zakuya kupambana kuya kwa manda, nanga ungadziwe chiyani? (Sheol )
(parallel missing)
“Aa, Inu mukanangondibisa mʼmanda ndi kundiphimba kuti ndisaoneke mpaka mkwiyo wanu utapita! Achikhala munandiyikira nthawi, kuti pambuyo pake mundikumbukirenso. (Sheol )
(parallel missing)
Ngati nyumba imene ndikuyiyembekezera ndi manda, ngati ndiyala bedi langa mu mdima, (Sheol )
(parallel missing)
Ndithu sindidzakhalanso ndi chiyembekezo chilichonse, polowa mʼmanda, pamene ndidzatsikira ku fumbi.” (Sheol )
(parallel missing)
Zaka zawo zimatha ali mu ulemerero ndipo amatsikira ku manda mwamtendere. (Sheol )
(parallel missing)
Monga momwe kutentha ndi chilala zimasungunulira madzi owundana ndi momwemonso mmene manda amachotsera omwe achimwa. (Sheol )
(parallel missing)
Dziko la anthu akufa ndi lapululu pamaso pa Mulungu; chiwonongeko ndi chosaphimbidwa. (Sheol )
(parallel missing)
Palibe amene amakukumbukirani pamene wamwalira; Amakutamandani ndani ali ku manda? (Sheol )
(parallel missing)
Oyipa amabwerera ku manda, mitundu yonse imene imayiwala Mulungu. (Sheol )
(parallel missing)
chifukwa Inu simudzandisiya ku manda, simudzalola kuti woyera wanu avunde. (Sheol )
(parallel missing)
Anandimanga ndi zingwe za ku manda; misampha ya imfa inalimbana nane. (Sheol )
(parallel missing)
Inu Yehova, munanditulutsa ku manda, munandisunga kuti ndisatsalire mʼdzenje. (Sheol )
(parallel missing)
Yehova musalole kuti ndichite manyazi, pakuti ndalirira kwa Inu; koma oyipa achititsidwe manyazi ndipo agone chete mʼmanda. (Sheol )
(parallel missing)
Monga nkhosa iwo ayenera kupita ku manda, ndipo imfa idzawadya. Olungama adzawalamulira mmawa; matupi awo adzavunda mʼmanda, kutali ndi nyumba zawo zaufumu. (Sheol )
(parallel missing)
Koma Mulungu adzawombola moyo wanga kuchoka ku manda; ndithu Iye adzanditengera kwa Iye mwini. (Sheol )
(parallel missing)
Mulole imfa itenge adani anga mwadzidzidzi; alowe mʼmanda ali amoyo pakuti choyipa chili pakati pawo. (Sheol )
(parallel missing)
Pakuti chikondi chanu nʼchachikulu kwa ine; mwandipulumutsa ku malo ozama a manda. (Sheol )
(parallel missing)
Pakuti ndili ndi mavuto ambiri ndipo moyo wanga ukuyandikira ku manda. (Sheol )
(parallel missing)
Kodi ndi munthu uti angakhale ndi moyo ndi kusaona imfa? Kapena kudzipulumutsa yekha ku mphamvu ya manda? (Sela) (Sheol )
(parallel missing)
Zingwe za imfa zinandizinga, zoopsa za ku dziko la anthu akufa zinandigwera; ndinapeza mavuto ndi chisoni. (Sheol )
(parallel missing)
Ndikakwera kumwamba, Inu muli komweko; ndikakagona ku malo a anthu akufa, Inu muli komweko. (Sheol )
(parallel missing)
Iwo adzati, “Monga momwe nkhuni zimamwazikira akaziwaza, ndi momwenso mafupa athu amwazikira pa khomo la manda.” (Sheol )
(parallel missing)
tiwameze amoyo ngati manda, ndi athunthu ngati anthu otsikira mʼdzenje. (Sheol )
(parallel missing)
Mapazi ake amatsikira ku imfa; akamayenda ndiye kuti akupita ku manda. (Sheol )
(parallel missing)
Nyumba yake ndi njira yopita ku manda, yotsikira ku malo a anthu akufa. (Sheol )
(parallel missing)
Koma amunawo sadziwa kuti akufa ali kale komweko, ndi kuti alendo ake alowa kale mʼmanda akuya. (Sheol )
(parallel missing)
Manda ndi chiwonongeko ndi zosabisika pamaso pa Yehova, nanji mitima ya anthu! (Sheol )
(parallel missing)
Munthu wanzeru amatsata njira yopita ku moyo kuti apewe malo okhala anthu akufa. (Sheol )
(parallel missing)
Ukamukwapula ndi tsatsa udzapulumutsa moyo wake. (Sheol )
(parallel missing)
Manda sakhuta, nawonso maso a munthu sakhuta. (Sheol )
(parallel missing)
Manda, mkazi wosabala, nthaka yosakhuta madzi ndiponso moto womangoyakirayakira!” (Sheol )
(parallel missing)
Ntchito iliyonse imene ukuyigwira, uyigwire ndi mphamvu zako zonse, pakuti ku manda kumene ukupita kulibe kugwira ntchito, kulibe malingaliro, chidziwitso ndiponso nzeru. (Sheol )
(parallel missing)
Undiyike pamtima pako ngati chidindo, ngati chidindo cha pa dzanja lako; pakuti chikondi nʼchamphamvu ngati imfa, nsanje ndiyaliwuma ngati manda. Chikondi chimachita kuti lawilawi ngati malawi a moto wamphamvu. (Sheol )
(parallel missing)
Nʼchifukwa chake ku manda sikukhuta ndipo kwayasama kwambiri kukamwa kwake; mʼmandamo mudzagweranso anthu otchuka a mu Yerusalemu pamodzi ndi anthu wamba ochuluka; adzagweramo ali wowowo, nʼkuledzera kwawoko. (Sheol )
(parallel missing)
“Pempha chizindikiro kwa Yehova Mulungu wako, chikhale chozama ngati manda kapena chachitali ngati mlengalenga.” (Sheol )
(parallel missing)
Ku manda kwatekeseka kuti akulandire ukamabwera; mizimu ya anthu akufa, aja amene anali atsogoleri a dziko lapansi, yadzutsidwa. Onse amene anali mafumu a mitundu ya anthu ayimiritsidwa pa mipando yawo. (Sheol )
(parallel missing)
Ulemerero wako wonse walowa mʼmanda, pamodzi ndi nyimbo za azeze ako; mphutsi zayalana pogona pako ndipo chofunda chako ndi nyongolotsi. (Sheol )
(parallel missing)
Koma watsitsidwa mʼmanda pansi penipeni pa dzenje. (Sheol )
(parallel missing)
Inu mumayankhula monyada kuti, “Ife tinachita pangano ndi imfa, ife tachita mgwirizano ndi manda. Pamene mliri woopsa ukadzafika sudzatikhudza ife, chifukwa timadalira bodza ngati pothawirapo pathu ndi chinyengo ngati malo anthu obisalapo.” (Sheol )
(parallel missing)
Pangano limene munachita ndi imfa lidzathetsedwa; mgwirizano wanu ndi manda udzachotsedwa. Pakuti mliri woopsa udzafika, ndipo udzakugonjetsani. (Sheol )
(parallel missing)
Ine ndinaganiza kuti ndidzapita ku dziko la akufa pamene moyo ukukoma. (Sheol )
(parallel missing)
Pakuti akumanda sangathe kukutamandani, akufa sangayimbe nyimbo yokutamandani. Iwo amene akutsikira ku dzenje sangakukhulupirireni. (Sheol )
(parallel missing)
Mumapita kukapembedza fano la Moleki mutatenga mafuta ndi zonunkhira zochuluka. Munachita kutumiza akazembe anu kutali; inu ngakhale munapita ku manda kwenikweniko! (Sheol )
(parallel missing)
“‘Ine Ambuye Yehova ndikuti: Pa nthawi imene mkungudzawo unatsikira ku manda, ndinawuza nyanja kuti iwulire maliro pakuwuphimba. Ndinawumitsa mitsinje ndipo madzi ambiri anaphwa. Ndinabweretsa mdima pa Lebanoni chifukwa cha mtengowo ndipo mitengo yonse ya mʼdzikomo inawuma. (Sheol )
(parallel missing)
Mitundu ya anthu inagwedezeka pakumva mkokomo wa kugwa kwake, pamene ndinawutsitsira ku manda pamodzi ndi iwo amene anafa. Pamenepo ku dziko la akufa mitengo yonse ya ku Edeni pamodzi ndi ya ku Lebanoni yosankhidwa bwino inasangalatsidwa chifukwa cha zimenezi. (Sheol )
(parallel missing)
Amene ankakhala mu mthunzi wake, amene ankayanjana nawo, iwonso anapita nawo pamodzi ku manda, kukakhala pamodzi ndi amene anaphedwa ndi lupanga pakati pa mitundu ya anthu. (Sheol )
(parallel missing)
Mʼkati mwa manda atsogoleri amphamvu pamodzi ndi ogwirizana nawo azidzakambirana za Igupto nʼkumati, ‘Afika kuno anthu osachita mdulidwe aja! Ndi awa agona apawa, ophedwa pa nkhondo.’ (Sheol )
(parallel missing)
Iwo sanayikidwe mwaulemu ngati ankhondo amphamvu amakedzana, amene anatsikira ku dziko la anthu akufa ndi zida zawo zomwe za nkhondo. Malupanga awo anawayika ku mitu yawo, ndipo zishango zawo anaphimba mafupa awo. Kale anthu amphamvu amenewa ankaopsa dziko la anthu amoyo. (Sheol )
(parallel missing)
“Ndidzawapulumutsa ku mphamvu ya manda; ndidzawawombola ku imfa. Kodi iwe imfa, miliri yako ili kuti? Kodi iwe manda, kuwononga kwako kuli kuti? “Sindidzachitanso chifundo, (Sheol )
(parallel missing)
Ngakhale atakumba pansi mpaka ku malo a anthu akufa, dzanja langa lidzawatulutsa kumeneko. Ngakhale atakwera kumwamba Ine ndidzawatsakamutsa kumeneko. (Sheol )
(parallel missing)
Iye anati: “Pamene ndinali mʼmavuto anga ndinayitana Yehova, ndipo Iye anandiyankha. Ndili ku dziko la anthu akufa ndinapempha thandizo, ndipo Inu munamva kulira kwanga. (Sheol )
(parallel missing)
Ndithu, wasokonezeka ndi vinyo; ndi wodzitama ndiponso wosakhazikika. Pakuti ngodzikonda ngati manda, ngosakhutitsidwa ngati imfa, wadzisonkhanitsira mitundu yonse ya anthu ndipo wagwira ukapolo anthu a mitundu yonse. (Sheol )
(parallel missing)
Koma Ine ndikukuwuzani kuti aliyense wokwiyira mʼbale wake adzapezeka wolakwa ku bwalo la milandu. Ndiponso aliyense amene wonena mʼbale wake kuti, ‘Ndiwe wopanda phindu,’ adzapezeka wolakwa ku bwalo la milandu lalikulu. Ndipo aliyense amene anganene mnzake ‘wopandapake’ adzatengeredwa ku bwalo la milandu. Ndiponso aliyense amene angamunene mnzake kuti, ‘Chitsiru iwe,’ adzaponyedwa ku gehena. (Geenna )
Dar Eu vă spun că oricine se mânie pe fratele său fără motiv va fi în primejdie de judecată. Oricine îi va spune fratelui său: “Raca!” va fi în pericol de consiliu. Oricine îi va spune: “Prostule!” va fi în pericol de focul gheenei. (Geenna )
Ngati diso lako lakumanja likuchimwitsa, ulichotse ndi kulitaya. Pakuti nʼkwabwino kwa iwe kutaya chiwalo chimodzi cha thupi lako, kusiyana ndi kuti thupi lonse liponyedwe mʼgehena. (Geenna )
Dacă ochiul tău drept te face să te poticnești, smulge-l și aruncă-l de la tine. Căci este mai de folos să piară unul dintre membrele tale decât ca tot trupul tău să fie aruncat în gheenă. (Geenna )
Ndipo ngati dzanja lako lamanja likuchimwitsa, ulidule ndi kulitaya. Pakuti nʼkwabwino kwa iwe kutaya chiwalo chimodzi cha thupi lako, kusiyana ndi kuti thupi lonse liponyedwe mʼgehena. (Geenna )
Dacă mâna ta dreaptă te face să te poticnești, taie-o și arunc-o departe de tine. Căci îți este mai de folos să piară unul din membrele tale, decât să fie aruncat tot trupul tău în Gheenă. (Geenna )
Musamaope amene amapha thupi koma sangathe kuchotsa moyo. Koma muziopa Iye amene akhoza kupha mzimu ndi kuwononga thupi mu gehena. (Geenna )
Nu vă temeți de cei care ucid trupul, dar nu pot ucide sufletul. Temeți-vă mai degrabă de cel care este în stare să nimicească și sufletul și trupul în Gheenă. (Geenna )
Ndipo iwe Kaperenawo, kodi udzakwezedwa kufika kumwamba? Ayi, udzatsitsidwa mpaka pansi kufika ku Hade. Ngati zodabwitsa zimene zinachitika mwa iwe, zikanachitika mu Sodomu, bwenzi iye alipo kufikira lero. (Hadēs )
Tu, Capernaum, care te-ai înălțat la cer, te vei coborî în Hades. Căci, dacă s-ar fi făcut în Sodoma lucrările mărețe care s-au făcut în voi, ar fi rămas până astăzi. (Hadēs )
Aliyense amene anena mawu otsutsana ndi Mwana wa Munthu adzakhululukidwa koma aliyense wonena motsutsana ndi Mzimu Woyera sadzakhululukidwa mu mʼbado uno kapena umene ukubwerawo. (aiōn )
Oricine va spune un cuvânt împotriva Fiului Omului, îi va fi iertat, dar oricine va vorbi împotriva Duhului Sfânt, nu-i va fi iertat, nici în veacul acesta, nici în cel viitor. (aiōn )
Zimene zinafesedwa pakati pa minga, ndi munthu amene amamva mawu koma nkhawa za moyo uno ndi chinyengo cha chuma zimalepheretsa mawuwo kuti abale chipatso. (aiōn )
Ceea ce a fost semănat între spini, acesta este cel care ascultă cuvântul, dar grijile veacului acestuia și înșelăciunea bogățiilor înăbușă cuvântul, și el devine neînsuflețit. (aiōn )
Ndipo amene anafesa namsongole ndi Satana. Kukolola ndiko kutha kwa dzikoli ndipo otuta ndi angelo. (aiōn )
Dușmanul care le-a semănat este diavolul. Secerișul este sfârșitul veacului, iar secerătorii sunt îngerii. (aiōn )
“Monga momwe namsongole azulidwa ndi kutenthedwa ndi moto, momwemonso kudzakhala pakutha kwa dziko. (aiōn )
De aceea, așa cum buruienile de scorbură sunt adunate și arse în foc, așa va fi și la sfârșitul acestui veac. (aiōn )
Umu ndi mmene kudzakhalira pakutha kwa dziko. Angelo adzabwera ndi kulekanitsa oyipa ndi olungama. (aiōn )
Așa va fi și la sfârșitul lumii. Îngerii vor veni și îi vor despărți pe cei răi dintre cei drepți (aiōn )
Ndipo Ine ndikuwuza iwe kuti ndiwe Petro ndipo pa thanthwe ili Ine ndidzamangapo mpingo wanga ndipo makomo a ku gehena sadzawugonjetsa. (Hadēs )
Îți spun și Eu îți spun că tu ești Petru și pe această piatră voi zidi Adunarea Mea și porțile Hadesului nu o vor birui. (Hadēs )
Ngati dzanja lako kapena phazi lako likuchimwitsa, lidule ndi kulitaya. Ndi bwino kwa iwe kulowa mʼmoyo wosatha wolumala kusiyana ndi kukhala ndi manja awiri kapena mapazi awiri ndi kukaponyedwa ku moto wosatha. (aiōnios )
Dacă mâna sau piciorul tău te face să te poticnești, taie-le și leapădă-le de la tine. Este mai bine pentru tine să intri în viață mutilat sau schilodit, decât să ai două mâini sau două picioare pentru a fi aruncat în focul veșnic. (aiōnios )
Ndipo ngati diso lako likuchimwitsa, ulichotse ndi kulitaya. Ndi bwino kwa iwe kuti ukalowe ku moyo wosatha ndi diso limodzi kuposa ndi kukhala ndi maso awiri ndi kukaponyedwa ku moto wa gehena.” (Geenna )
Dacă ochiul tău te face să te poticnești, smulge-l și aruncă-l de la tine. Este mai bine pentru tine să intri în viață cu un singur ochi, decât să ai doi ochi pentru a fi aruncat în gheena de foc. (Geenna )
Taonani mnyamata wina anabwera kwa Yesu namufunsa kuti, “Aphunzitsi, ndi chinthu chiti chabwino chimene ndiyenera kuchita kuti ndipeze moyo wosatha?” (aiōnios )
Și iată că a venit cineva la El și a zis: “Învățătorule, ce să fac ca să am viața veșnică?” (aiōnios )
Ndipo aliyense amene wasiya nyumba, kapena abale, kapena alongo, kapena bambo kapena mayi kapena mkazi, kapena ana, kapena minda chifukwa cha Ine adzalandira madalitso ochuluka ndi kulandiranso moyo wosatha. (aiōnios )
Oricine a lăsat case, sau frați, sau surori, sau tată, sau mamă, sau soție, sau copii, sau pământuri, de dragul numelui Meu, va primi de o sută de ori și va moșteni viața veșnică. (aiōnios )
Ataona mtengo wamkuyu mʼmbali mwa msewu, anapitapo koma sanapeze kanthu koma masamba okhaokha. Pamenepo anati kwa mtengowo, “Usadzabalenso chipatso!” Nthawi yomweyo mtengowo unafota. (aiōn )
Văzând un smochin lângă drum, s-a apropiat de el și n-a găsit pe el decât frunze. I-a spus: “Să nu mai fie niciun fruct de la tine în veci!” Imediat smochinul s-a uscat. (aiōn )
“Tsoka kwa inu, aphunzitsi amalamulo ndi Afarisi, achiphamaso! Mumayenda maulendo ambiri pa mtunda ndi pa nyanja kuti mutembenuze munthu mmodzi, ndipo akatembenuka, mumamusandutsa kukhala mwana wa gehena kawiri kuposa inu. (Geenna )
Vai vouă, cărturari și farisei, ipocriților! Pentru că voi călătoriți pe mare și pe uscat ca să faceți un singur proselit; și când acesta devine unul, îl faceți de două ori mai fiu al Gheenei decât voi înșivă. (Geenna )
“Njoka inu! Ana amamba! Mudzachithawa bwanji chilango cha gehena? (Geenna )
Voi, șerpi, urmași ai viperelor, cum veți scăpa de judecata Gheenei? (Geenna )
Pamene Yesu anakhala pansi pa phiri la Olivi, ophunzira ake anabwera kwa Iye mwamseri nati, “Tiwuzeni, kodi izi zidzachitika liti, ndipo chizindikiro cha kubwera kwanu ndi zizindikiro za kutha kwa dziko zidzakhala chiyani?” (aiōn )
Pe când ședea El pe Muntele Măslinilor, ucenicii au venit la El în particular și I-au zis: “Spune-ne, când se vor întâmpla aceste lucruri? Care este semnul venirii Tale și al sfârșitului veacului?” (aiōn )
“Pamenepo adzanena kwa akumanzere kwake kuti, ‘Chokani kwa Ine, inu otembereredwa, pitani ku moto wosatha wokonzedwera mdierekezi ndi angelo ake. (aiōnios )
Apoi va spune și celor de la stânga: 'Duceți-vă de la Mine, blestemaților, în focul cel veșnic, pregătit diavolului și îngerilor lui; (aiōnios )
“Amenewa adzapita ku chilango chosatha pamene olungama ku moyo wosatha.” (aiōnios )
Aceștiavor pleca la pedeapsa veșnică, dar cei drepți la viața veșnică.” (aiōnios )
ndi kuwaphunzitsa amvere zonse zimene ndinakulamulirani. Ndipo onani, Ine ndidzakhala pamodzi ndi inu kufikira kutha kwa dziko lapansi pano.” (aiōn )
învățându-isă păzească toate lucrurile pe care vi le-am poruncit. Iată, Eu sunt cu voi în toate zilele, până la sfârșitul veacului.” Amin. (aiōn )
koma aliyense amene achitira mwano Mzimu Woyera sadzakhululukidwa pakuti wachita tchimo losatha.” (aiōn , aiōnios )
dar oricine va huli împotriva Duhului Sfânt nu va avea iertare, ci va fi supus osândei veșnice.” (aiōn , aiōnios )
koma nkhawa zamoyo uno, chinyengo cha chuma ndi zokhumba za zinthu zina zimabwera ndi kutchinga mawu, ndipo amawachititsa kukhala osabala chipatso. (aiōn )
dar grijile acestui veac, înșelăciunea bogățiilor și poftele altor lucruri care intră în el înăbușă cuvântul și acesta devine neînsuflețit. (aiōn )
Ngati dzanja lako likuchimwitsa, lidule. Ndi kwabwino kwa iwe kulowa mʼmoyo ndi dzanja limodzi kusiyana ndi kukhala ndi manja awiri ndi kupita ku gehena, kumene moto wake suzima. (Geenna )
Dacă mâna ta te face să te poticnești, taie-ți-o! Este mai bine pentru tine să intri în viață mutilat, decât să ai cele două mâini pentru a merge în Gheena, în focul nestins, (Geenna )
Ndipo ngati phazi lako likuchimwitsa, lidule. Ndi kwabwino kwa iwe kulowa mʼmoyo olumala kusiyana ndi kukhala ndi mapazi awiri ndi kuponyedwa mu gehena. (Geenna )
Dacă piciorul tău te face să te poticnești, taie-l! Este mai bine pentru tine să intri în viață șchiop, decât ca cele două picioare să fie aruncate în Gheena, în focul care nu se va stinge niciodată — (Geenna )
Ndipo ngati diso lako likuchimwitsa, likolowole. Ndi kwabwino kwa iwe kulowa ufumu wa Mulungu ndi diso limodzi, kusiyana ndi kukhala ndi maso awiri ndi kuponyedwa mu gehena, (Geenna )
Dacă ochiul tău te face să te poticnești, aruncă-l afară. Este mai bine pentru tine să intri în Împărăția lui Dumnezeu cu un singur ochi, decât să ai doi ochi pentru a fi aruncat în Gheena de foc, (Geenna )
Yesu atanyamuka, munthu wina anamuthamangira nagwa mogwada pamaso pake. Iye anafunsa kuti, “Aphunzitsi abwino, ndichite chiyani kuti ndilandire moyo wosatha?” (aiōnios )
Pe când ieșea El pe cale, a alergat unul la El, a îngenuncheat înaintea Lui și L-a întrebat: “Învățătorule, ce să fac ca să moștenesc viața veșnică?” (aiōnios )
adzalephera kulandira 100 (nyumba, abale, alongo, amayi, ana ndi minda, pamodzi ndi mazunzo) mʼbado uno ndi moyo wosatha nthawi ya mʼtsogolo. (aiōn , aiōnios )
ci va primi de o sută de ori mai mult acum, în veacul acesta: case, frați, surori, mame, copii, pământ, cu prigoane, iar în veacul viitor, viața veșnică. (aiōn , aiōnios )
Ndipo Iye anati kwa mtengo, “Palibe amene adzadyenso chipatso kuchokera kwa iwe.” Ndipo ophunzira ake anamva Iye akunena izi. (aiōn )
Isus i-a spus: “Fie ca nimeni să nu mai mănânce vreodată fructe de la tine!”, iar discipolii lui au auzit. (aiōn )
ndipo adzalamulira pa nyumba ya Yakobo ku nthawi zonse; ufumu wake sudzatha.” (aiōn )
și va domni peste casa lui Iacov pentru totdeauna. Împărăția lui nu va avea sfârșit”. (aiōn )
Kwa Abrahamu ndi zidzukulu zake ku nthawi zonse monga ananena kwa makolo athu.” (aiōn )
așa cum a vorbit părinților noștri, lui Avraam și urmașilor lui în veci.” (aiōn )
(Monga mmene ananenera kudzera mwa aneneri oyera), (aiōn )
(așa cum a vorbit prin gura sfinților Săi prooroci care au fost din vechime), (aiōn )
Ndipo ziwandazo zimamupempha mobwerezabwereza kuti asazitumize ku dzenje la mdima. (Abyssos )
Ei l-au implorat să nu le poruncească să se ducă în abis. (Abyssos )
Kodi iwe Kaperenawo, adzakukweza mpaka kumwamba? Ayi, adzakutsitsa mpaka ku Malo a anthu akufa. (Hadēs )
Tu, Capernaum, care te-ai înălțat la cer, vei fi coborât în Hades. (Hadēs )
Nthawi ina katswiri wa malamulo anayimirira kuti ayese Yesu. Iye anati, “Aphunzitsi, ndichite chiyani kuti ndikhale ndi moyo wosatha?” (aiōnios )
Și iată că un învățător s-a ridicat în picioare și L-a pus la încercare, zicând: “Învățătorule, ce să fac ca să moștenesc viața veșnică?” (aiōnios )
Koma Ine ndidzakuonetsani amene muyenera kumuopa: Wopani Iye, amene pambuyo pakupha thupi, ali ndi mphamvu yakukuponyani ku gehena. Inde, Ine ndikuwuzani, muopeni Iye. (Geenna )
Ci vă voi avertiza de cine trebuie să vă temeți. Temeți-vă de cel care, după ce a ucis, are puterea de a arunca în Gheenă. Da, vă spun, temeți-vă de el. (Geenna )
“Bwana anayamikira kapitawo wosakhulupirikayo popeza anachita mochenjera. Pakuti anthu a dziko lino lapansi ndi ochenjera kwambiri akamachita zinthu ndi anthu ofanana nawo kuposa anthu a kuwunika. (aiōn )
“Domnul său l-a lăudat pe administratorul necinstit pentru că a procedat cu înțelepciune, căci copiii acestei lumi sunt, în neamul lor, mai înțelepți decât copiii luminii. (aiōn )
Ine ndikukuwuzani inu, gwiritsani ntchito chuma cha dziko lapansi kuti mudzipezere nokha abwenzi, kuti pamene chatha mudzalandiridwe mʼmalo okhala amuyaya. (aiōnios )
Eu vă spun: faceți-vă prieteni prin intermediul bogățiilor nedrepte, pentru ca, atunci când veți eșua, ei să vă primească în corturile veșnice. (aiōnios )
Ali mʼgehena kuzunzika, anakweza maso ake ndipo anaona Abrahamu ali ndi Lazaro pambali pake. (Hadēs )
În Hades, și-a ridicat ochii, fiind în chinuri, și a văzut departe pe Avraam și pe Lazăr la sânul lui. (Hadēs )
Oweruza wina wake anamufunsa Iye kuti, “Aphunzitsi abwino, ndichite chiyani kuti ndilandire moyo wosatha?” (aiōnios )
Un domnitor L-a întrebat: “Învățătorule, ce să fac ca să moștenesc viața veșnică?” (aiōnios )
adzalephera kulandira mowirikiza mʼmoyo uno, ndi mʼmoyo ukubwerawo, moyo wosatha.” (aiōn , aiōnios )
care să nu primească de multe ori mai mult în acest timp și în lumea viitoare viața veșnică.” (aiōn , aiōnios )
Yesu anayankha kuti, “Anthu a mʼbado uno amakwatira ndi kukwatiwa. (aiōn )
Isus le-a zis: “Copiii veacului acestuia se căsătoresc și sunt dați în căsătorie. (aiōn )
Koma mʼmoyo umene ukubwerawo, anthu amene adzaukitsidwe kwa akufa sadzakwatira kapena kukwatiwa. (aiōn )
Dar cei care sunt considerați vrednici să ajungă la vârsta aceea și la învierea din morți nu se căsătoresc și nici nu sunt dați în căsătorie. (aiōn )
kuti aliyense amene akhulupirira Iye akhale ndi moyo wosatha. (aiōnios )
pentru ca oricine crede în el să nu piară, ci să aibă viață veșnică. (aiōnios )
“Pakuti Mulungu anakonda dziko lapansi, kotero anapereka Mwana wake wobadwa yekha, kuti aliyense wokhulupirira Iye asatayike koma akhale ndi moyo wosatha. (aiōnios )
Fiindcă atât de mult a iubit Dumnezeu lumea, încât a dat pe singurul Său Fiu născut, pentru ca oricine crede în El să nu piară, ci să aibă viață veșnică. (aiōnios )
Aliyense wokhulupirira Mwanayo ali ndi moyo wosatha, koma iye amene samvera Mwanayo sadzawuona moyo, pakuti mkwiyo wa Mulungu umakhala pa iye.” (aiōnios )
Cine crede în Fiul are viață veșnică, dar cine nu ascultă de Fiul nu va vedea viața, ci mânia lui Dumnezeu rămâne asupra lui.” (aiōnios )
koma aliyense amene adzamwa madzi amene Ine ndidzamupatsa sadzamvanso ludzu. Ndithudi, madzi amene ndidzamupatsa adzakhala kasupe wamadzi wotumphukira ku moyo wosatha.” (aiōn , aiōnios )
dar oricine va bea din apa pe care i-o voi da Eu, nu va mai înseta niciodată, ci apa pe care i-o voi da Eu va deveni în el un izvor de apă care izvorăște pentru viața veșnică.” (aiōn , aiōnios )
Ngakhale tsopano amene akukolola akulandira malipiro ake, ndipo akututa mbewu ku moyo wosatha kuti wofesa ndi wokolola asangalale pamodzi. (aiōnios )
Cel care seceră primește plata și culege roade pentru viața veșnică, pentru ca atât cel care seamănă, cât și cel care seceră să se bucure împreună. (aiōnios )
“Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti aliyense amene amamva mawu anga ndi kukhulupirira Iye amene ananditumiza Ine, ali ndi moyo wosatha ndipo sadzaweruzidwa. Iye wachoka mu imfa ndipo walowa mʼmoyo. (aiōnios )
“Adevărat vă spun că cine ascultă cuvântul Meu și crede pe Cel ce M-a trimis pe Mine are viață veșnică și nu vine la judecată, ci a trecut din moarte la viață. (aiōnios )
Inu mumasanthula malemba chifukwa mumaganiza kuti mʼmalembamo muli moyo wosatha. Awa ndi malemba amene akundichitira umboni. (aiōnios )
Voi cercetați Scripturile, pentru că credeți că în ele aveți viața veșnică; și acestea sunt cele ce mărturisesc despre Mine. (aiōnios )
Gwirani ntchito, osati chifukwa cha chakudya chimene chimawonongeka koma chifukwa cha chakudya chimene sichiwonongeka mpaka ku moyo wosatha, chimene Mwana wa Munthu adzakupatsani. Mulungu Atate anamusindikiza chizindikiro chomuvomereza.” (aiōnios )
Nu lucrați pentru hrana care piere, ci pentru hrana care rămâne pentru viața veșnică, pe care v-o va da Fiul Omului. Căci Dumnezeu Tatăl l-a pecetluit.” (aiōnios )
Pakuti chifuniro cha Atate anga ndi chakuti aliyense amene aona Mwanayo namukhulupirira akhale ndi moyo wosatha, ndipo Ine ndidzamuukitsa kwa akufa pa tsiku lomaliza.” (aiōnios )
Aceasta este voia Celui care m-a trimis: ca oricine vede pe Fiul și crede în El să aibă viața veșnică; și Eu îl voi învia în ziua de apoi.” (aiōnios )
Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti Iye amene akhulupirira ali nawo moyo wosatha. (aiōnios )
Adevărat, vă spun, cel ce crede în Mine are viața veșnică. (aiōnios )
Ine ndine chakudya chamoyo chochokera kumwamba. Ngati munthu adya chakudya ichi, adzakhala ndi moyo nthawi zonse. Chakudya chimenechi ndi thupi langa, limene Ine ndidzalipereka kuti anthu pa dziko lapansi akhale ndi moyo.” (aiōn )
Eu sunt pâinea vie care s-a coborât din cer. Dacă cineva mănâncă din pâinea aceasta, va trăi în veci. Da, pâinea pe care o voi da pentru viața lumii este carnea mea.” (aiōn )
Aliyense amene adya thupi langa ndi kumwa magazi anga ali ndi moyo wosatha ndipo Ine ndidzamuukitsa kwa akufa pa tsiku lomaliza. (aiōnios )
Cine mănâncă carnea Mea și bea sângele Meu are viață veșnică și Eu îl voi învia în ziua de apoi. (aiōnios )
Ichi ndiye chakudya chimene chinatsika kuchokera kumwamba. Makolo athu akale anadya mana ndi kufa, koma iye amene adya chakudya ichi, adzakhala ndi moyo nthawi yonse.” (aiōn )
Aceasta este pâinea care s-a coborât din cer — nu cum au mâncat părinții noștri mana și au murit. Cel care mănâncă această pâine va trăi în veci.” (aiōn )
Simoni Petro anamuyankha Iye kuti, “Ambuye, ife tidzapita kwa yani? Inu muli ndi mawu amoyo wosatha. (aiōnios )
Simon Petru I-a răspuns: “Doamne, la cine să mergem? Tu ai cuvintele vieții veșnice. (aiōnios )
Pajatu kapolo alibe malo wokhazikika mʼbanja, koma mwana ndi wa mʼbanjamo nthawi zonse. (aiōn )
O roabă nu locuiește în casă pentru totdeauna. Un fiu rămâne pentru totdeauna. (aiōn )
Ine ndikukuwuzani choonadi, munthu akasunga mawu anga, sadzafa konse.” (aiōn )
Mai mult ca sigur, vă spun că, dacă o persoană respectă cuvântul meu, nu va vedea niciodată moartea.” (aiōn )
Pamenepo Ayuda anafuwula kuti, “Tsopano ife tadziwadi kuti Inu ndi wogwidwa ndi chiwanda! Abrahamu anafa ndiponso aneneri, koma Inu mukunena kuti, ‘Ngati munthu asunga mawu anga, sadzafa.’ (aiōn )
Atunci iudeii i-au zis: “Acum știm că ai un demon. Avraam a murit, ca și profeții, iar tu spui: “Dacă un om păzește cuvântul Meu, nu va gusta niciodată moartea”. (aiōn )
Palibe amene anamvapo za kutsekula maso a munthu wobadwa wosaona. (aiōn )
De la începutul lumii nu s-a auzit niciodată ca cineva să fi deschis ochii unui orb din naștere. (aiōn )
Ine ndimazipatsa moyo wosatha ndipo sizidzawonongeka. Palibe amene adzazikwatula mʼdzanja langa. (aiōn , aiōnios )
Eu le dau viața veșnică. Ele nu vor pieri niciodată și nimeni nu le va smulge din mâna mea. (aiōn , aiōnios )
Aliyense amene ali ndi moyo ndi kukhulupirira Ine sadzamwalira. Kodi iwe ukukhulupirira izi?” (aiōn )
Oricine trăiește și crede în Mine nu va muri niciodată. Crezi tu asta?” (aiōn )
Munthu amene amakonda moyo wake adzawutaya, pamene munthu amene amadana ndi moyo wake mʼdziko lino lapansi adzawusungira ku moyo wosatha. (aiōnios )
Cine își iubește viața o va pierde. Cel care își urăște viața în lumea aceasta o va păstra pentru viața veșnică. (aiōnios )
Gulu la anthu linayankha kuti, “Ife tinamva kuchokera mʼmalamulo kuti Khristu adzakhala kwamuyaya, nanga bwanji Inu mukunena kuti, ‘Mwana wa Munthu ayenera kukwezedwa?’ Kodi Mwana wa Munthuyu ndani?” (aiōn )
Și mulțimea i-a răspuns: “Am auzit din Lege că Hristosul rămâne pentru totdeauna. Cum spuneți voi: 'Fiul Omului trebuie să fie înălțat'? Cine este acest Fiu al Omului?” (aiōn )
Ine ndikudziwa kuti lamulo lake ndi moyo wosatha. Choncho chilichonse chimene Ine ndinena ndi chimene Atate andiwuza.” (aiōnios )
Știu că porunca Lui este viața veșnică. Așadar, lucrurile pe care le spun, așa cum mi-a spus Tatăl, așa vorbesc și eu.” (aiōnios )
Petro anati, “Ayi, Inu simudzandisambitsa konse mapazi anga.” Yesu anayankha kuti, “Ngati Ine sindisambitsa mapazi ako, ulibe gawo mwa Ine.” (aiōn )
Petru i-a zis: “Nu-mi vei spăla niciodată picioarele!” Isus i-a răspuns: “Dacă nu te spăl, nu ai parte cu Mine”. (aiōn )
Ine ndidzapempha Atate, ndipo adzakupatsani Nkhoswe ina kuti izikhala nanu nthawi zonse. (aiōn )
Eu mă voi ruga Tatălui și el vă va da un alt Sfetnic, ca să fie cu voi în veci: (aiōn )
Pakuti Inu munamupatsa Iye ulamuliro pa anthu onse kuti apereke moyo wosatha kwa onse amene mwamupatsa. (aiōnios )
așa cum i-ai dat autoritate peste toată făptura, așa va da viață veșnică tuturor celor pe care i-ai dat-o. (aiōnios )
Tsono moyo wosathawo ndi uwu: Iwo akudziweni Inu, Mulungu yekhayo woona, ndi Yesu Khristu, amene Inu mwamutuma. (aiōnios )
Aceasta este viața veșnică: să te cunoască pe tine, singurul Dumnezeu adevărat, și pe cel pe care l-ai trimis, Isus Hristos. (aiōnios )
Chifukwa simudzasiya moyo wanga kumalo a anthu akufa, ku manda, kapena kulekerera Woyerayo kuti awole. (Hadēs )
pentru că nu vei lăsa sufletul meu în Locuința morților, nici nu vei permite ca Sfântul tău să vadă putreziciunea. (Hadēs )
Davide ataoneratu zimene zinali mʼtsogolo anayankhula za kuuka kwa Khristu, kuti Iye sanasiyidwe mʼmanda, ndipo thupi lake silinawole. (Hadēs )
el, prevăzând acest lucru, a vorbit despre învierea lui Hristos, că sufletul lui nu a rămas în Hades și că trupul lui nu a văzut putrezirea. (Hadēs )
Iye ayenera kukhalabe kumwamba mpaka nthawi ya kukonzanso zinthu zonse monga Mulungu analonjeza kale kudzera mwa aneneri ake oyera mtima. (aiōn )
pe care cerul trebuie să-L primească până la vremurile de refacere a tuturor lucrurilor, pe care Dumnezeu le-a spus demult prin gura sfinților Săi prooroci. (aiōn )
Ndipo Paulo ndi Barnaba anawayankha molimba mtima kuti, “Ife tinayenera kuyankhula Mawu a Mulungu kwa inu poyamba. Popeza inu mwawakana ndi kudziyesa nokha osayenera moyo wosatha, ife tsopano tikupita kwa anthu a mitundu ina. (aiōnios )
Pavel și Barnaba au luat cuvântul cu îndrăzneală și au zis: “Trebuia să vă fie vestit mai întâi cuvântul lui Dumnezeu. Întrucât, într-adevăr, îl respingeți de la voi înșivă și vă judecați nevrednici de viața veșnică, iată că ne întoarcem la neamuri. (aiōnios )
Anthu a mitundu ina atamva izi, anakondwa ndipo analemekeza Mawu Ambuye; ndipo onse amene anawasankha kuti alandire moyo osatha anakhulupirira. (aiōnios )
Neamurile, auzind acestea, s-au bucurat și au slăvit cuvântul lui Dumnezeu. Toți cei care erau rânduiți pentru viața veșnică au crezut. (aiōnios )
zinaululidwa kuyambira kalekale.’ (aiōn )
“Toate lucrările lui Dumnezeu sunt cunoscute de El din veșnicie. (aiōn )
Pakuti kuyambira pamene dziko lapansi linalengedwa, zinthu zosaoneka za Mulungu, mphamvu zake zosatha ndi chikhalidwe cha umulungu, zakhala zikuoneka bwinobwino. Akhala akuzindikira poona zimene Mulungu analenga, kotero kuti anthu sangathe kuwiringula. (aïdios )
Căci lucrurile invizibile ale Lui, de la crearea lumii, se văd în mod clar, fiind percepute prin lucrurile care sunt făcute, adică puterea Lui veșnică și divinitatea Lui, pentru ca ei să fie fără scuză. (aïdios )
Iwo anasinthanitsa choonadi cha Mulungu ndi bodza ndipo anapembedza ndi kutumikira zinthu zolengedwa mʼmalo mwa Mlengi amene ali woyenera kutamandidwa mpaka muyaya. Ameni. (aiōn )
care au schimbat adevărul lui Dumnezeu cu minciuna și s-au închinat și au slujit mai degrabă creaturii decât Creatorului, care este binecuvântat în veci. Amin. (aiōn )
Iye adzapereka moyo wosatha kwa amene amafunafuna ulemerero, ulemu ndi moyo pochita ntchito zabwino mopirira. (aiōnios )
celor care, prin perseverența în binele făcut, caută gloria, onoarea și incoruptibilitatea, viața veșnică; (aiōnios )
Choncho monga momwe tchimo linkalamulira anthu ndi kubweretsa imfa pa iwo, chomwecho kunali koyenera kuti chisomo chilamulire pobweretsa chilungamo kwa anthu, ndi kuwafikitsa ku moyo wosatha mwa Yesu Khristu Ambuye athu. (aiōnios )
pentru ca, după cum păcatul a domnit în moarte, tot așa harul să domnească prin dreptate pentru viața veșnică, prin Isus Hristos, Domnul nostru. (aiōnios )
Koma tsopano pakuti inu mwamasulidwa ku tchimo ndipo mwasanduka akapolo a Mulungu, phindu lomwe mulipeza ndi kuyera mtima ndipo chotsatira chake ndi moyo wosatha. (aiōnios )
Dar acum, fiind eliberați de păcat și deveniți robi ai lui Dumnezeu, aveți rodul sfințirii și rezultatul vieții veșnice. (aiōnios )
Pakuti malipiro a tchimo ndi imfa, koma mphatso yaulere imene Mulungu amapereka ndi moyo wosatha mwa Khristu Yesu Ambuye athu. (aiōnios )
Căci plata păcatului este moartea, dar darul gratuit al lui Dumnezeu este viața veșnică în Hristos Isus, Domnul nostru. (aiōnios )
Awo ndi makolo athu. Kuchokera kwa iwo mʼthupi ndi kumene kunachokera makolo a Khristu Yesu amene ndi Mulungu wolamulira zinthu zonse, alemekezeke mpaka muyaya! Ameni. (aiōn )
din care sunt părinții și din care provine Cristos în ceea ce privește trupul, care este peste toate, Dumnezeu, binecuvântat în veci. Amin. (aiōn )
“kapena ‘Ndani adzatsikira ku dziko la anthu akufa?’” (ndiko, kukamutenga Khristu kwa akufa). (Abyssos )
sau: “Cine se va coborî în abis?” (adică să-l coboare pe Cristos); sau: “Cine se va coborî în abis?”. (adică să-l aducă pe Hristos din morți).” (Abyssos )
Pakuti Mulungu anasandutsa anthu onse a mʼndende ya kusamvera kuti Iye akaonetse chifundo kwa onse. (eleēsē )
Căci Dumnezeu i-a legat pe toți de neascultare, ca să aibă milă de toți. (eleēsē )
Pakuti zinthu zonse nʼzochokera kwa Iye, nʼzolengedwa ndi Iye ndipo zimabweretsa ulemerero kwa Iye. Kwa Iye kukhale ulemerero mpaka muyaya! Ameni. (aiōn )
Căci din El, prin El și pentru El sunt toate lucrurile. A lui să fie gloria în veci! Amin. (aiōn )
Musafanizidwenso ndi makhalidwe a dziko lino koma musandulike pokonzanso maganizo anu. Ndipo mudzadziwa ndi kuzindikira chifuniro chabwino cha Mulungu chomwe ndi chokondweretsa ndi changwiro. (aiōn )
Nu vă potriviți cu lumea aceasta, ci transformați-vă prin înnoirea minții voastre, ca să puteți dovedi care este voia lui Dumnezeu, bună, plăcută și desăvârșită. (aiōn )
Tsopano kwa Iye amene ali ndi mphamvu yokhazikitsa monga mwa uthenga wanga wabwino ndikulalikidwa kwa Yesu Khristu, monga mwa vumbulutso lachinsinsi chobisika kwa nthawi yayitali, (aiōnios )
Și acum, Celui ce poate să vă întărească, după Buna Vestire a mea și după propovăduirea lui Isus Hristos, după descoperirea tainei, care a fost ținută ascunsă în veacuri îndelungate, (aiōnios )
koma tsopano chavumbulutsidwa ndi kudziwika kudzera mʼMalemba a uneneri mwa lamulo la Mulungu wosatha, kuti mitundu yonse ikhulupirire ndi kumvera Iye, (aiōnios )
dar care acum s-a descoperit și, prin Scripturile profeților, după porunca Dumnezeului veșnic, a fost făcută cunoscută tuturor neamurilor, pentru ascultarea credinței, (aiōnios )
kwa Mulungu yekhayo wanzeru kukhale ulemerero kwamuyaya kudzera mwa Yesu Khristu! Ameni. (aiōn )
pentru singurul și înțeleptul Dumnezeu, prin Isus Hristos, căruia I se cuvine slava în veci! Amin. (aiōn )
Munthu wanzeru ali kuti? Munthu wozama ndi maphunziro ali kuti? Munthu wodziwa zakuya zamakono ali kuti? Kodi Mulungu sanazipusitse nzeru za dziko lapansi? (aiōn )
Unde este înțeleptul? Unde este scribul? Unde este cel care discută în acest veac? Oare nu a făcut Dumnezeu nebună înțelepciunea acestei lumi? (aiōn )
Komabe ife timayankhula uthenga wa nzeru kwa okhwima, koma osati ndi nzeru ya mʼbado uno kapena ya olamula a mʼbado uno, amene mphamvu yawo ikutha. (aiōn )
Noi însă vorbim cu înțelepciune printre cei maturi, dar nu cu înțelepciunea lumii acesteia și nici cu cea a conducătorilor lumii acesteia, care sunt pe cale de dispariție. (aiōn )
Ayi, ife timayankhula za nzeru yobisika ya Mulungu, nzeru imene inabisidwa ndipo imene Mulungu anatikonzera mu ulemerero wathu isanayambe nthawi. (aiōn )
Ci noi vorbim înțelepciunea lui Dumnezeu în taină, înțelepciunea care a fost ascunsă, pe care Dumnezeu a rânduit-o mai dinainte de lumi, pentru gloria noastră, (aiōn )
Palibe olamulira aliyense wa mʼbado uno amene anamumvetsetsa popeza anakamumvetsetsa sakanamupachika Ambuye wa ulemerero. (aiōn )
și pe care nu a cunoscut-o niciunul dintre conducătorii acestei lumi. Căci, dacă ar fi știut-o, nu L-ar fi răstignit pe Domnul slavei. (aiōn )
Choncho musadzinyenge. Ngati wina wa inu akuganiza kuti ndi wanzeru pa mulingo wa mʼbado uno, ayenera kukhala “wopusa” kuti athe kukhala wanzeru. (aiōn )
Nimeni să nu se înșele pe sine însuși. Dacă cineva crede că este înțelept între voi în lumea aceasta, să se facă nebun, ca să devină înțelept. (aiōn )
Nʼchifukwa chake ngati zimene ine ndimadya zichititsa mʼbale wanga kugwa mu tchimo, sindidzadyanso chakudyacho kuti mʼbaleyo ndisamuchimwitse. (aiōn )
De aceea, dacă mâncarea îl face pe fratele meu să se poticnească, nu voi mai mânca carne în veci, ca să nu-l fac pe fratele meu să se poticnească. (aiōn )
Zinthu izi zinawachitikira kuti zikhale chitsanzo ndipo zinalembedwa kuti zikhale chenjezo kwa ife, amene tiyandikira nthawi ya kutha kwa zonse. (aiōn )
Toate aceste lucruri li s-au întâmplat lor ca exemplu și au fost scrise pentru învățătura noastră, asupra cărora au venit sfârșiturile veacurilor. (aiōn )
“Iwe imfa, kupambana kwako kuli kuti? Iwe imfa, ululu wako uli kuti?” (Hadēs )
“Moarte, unde este înțepătura ta? Hades, unde este victoria ta?” (Hadēs )
Mulungu wa dziko lapansi anachititsa khungu anthu osakhulupirira, kuti asathe kuona kuwala kwa Uthenga Wabwino umene umaonetsa ulemerero wa Khristu, amene ndi chifaniziro cha Mulungu. (aiōn )
în care dumnezeul acestei lumi a orbit mințile celor necredincioși, pentru ca lumina Bunei Vestiri a slavei lui Cristos, care este chipul lui Dumnezeu, să nu răsară asupra lor. (aiōn )
Pakuti masautso athu ndi opepuka ndi a kanthawi, koma akutitengera ulemerero wamuyaya umene ndi wopambana kwambiri. (aiōnios )
Căci necazul nostru ușor, care este de moment, ne lucrează din ce în ce mai mult o greutate veșnică de glorie, (aiōnios )
Motero sitiyangʼana zinthu zimene ndi zooneka ndi maso, koma zinthu zimene ndi zosaoneka. Pakuti zimene zimaoneka ndi zosakhalitsa, koma zimene sizioneka ndi zamuyaya. (aiōnios )
în timp ce noi nu ne uităm la lucrurile care se văd, ci la cele care nu se văd. Căci lucrurile care se văd sunt vremelnice, dar lucrurile care nu se văd sunt veșnice. (aiōnios )
Popeza tikudziwa kuti ngati msasa wa dziko lapansi umene tikukhalamo uwonongeka, tili ndi nyumba yochokera kwa Mulungu, nyumba yamuyaya yakumwamba, osati yomangidwa ndi manja a anthu. (aiōnios )
Căci știm că, dacă se va desființa cortul nostru pământesc, avem o clădire de la Dumnezeu, o casă nefăcută de mână, veșnică, în ceruri. (aiōnios )
Paja analemba kuti, “Wopereka mphatso zake mowolowamanja kwa osauka, chilungamo chake chimanka mpaka muyaya.” (aiōn )
După cum este scris, “S-a împrăștiat în străinătate. El a dat săracilor. Neprihănirea Lui rămâne pentru totdeauna.” (aiōn )
Mulungu, Atate a Ambuye Yesu, amene tiyenera kumutamanda nthawi zonse, akudziwa kuti sindikunama. (aiōn )
Dumnezeul și Tatăl Domnului Isus Hristos, cel binecuvântat în veci de veci, știe că nu mint. (aiōn )
Yesuyo anadzipereka yekha chifukwa cha machimo athu kuti atipulumutse ku njira za moyo woyipa uno, molingana ndi chifuniro cha Mulungu ndi Atate athu. (aiōn )
care S-a dat pe Sine însuși pentru păcatele noastre, ca să ne izbăvească din veacul acesta rău, după voia Dumnezeului și Tatălui nostru, (aiōn )
Ulemerero ukhale kwa Mulunguyo mpaka muyaya. Ameni. (aiōn )
căruia I se cuvine slava în vecii vecilor. Amin. (aiōn )
Pakuti amene amafesa zokondweretsa thupi lake la uchimo, kuchokera ku khalidwe limenelo adzakolola chiwonongeko; amene amafesa zokondweretsa Mzimu, kuchokera kwa Mzimu adzakolola moyo wosatha. (aiōnios )
Căci cine seamănă pentru carnea sa, din carne va secera corupție. Dar cel care seamănă pentru Duhul va secera din Duhul viața veșnică. (aiōnios )
Anamukhazika pamwamba pa ulamuliro onse ndi mafumu, mphamvu ndi ufumu, ndiponso pamwamba pa dzina lililonse limene angalitchule, osati nthawi ino yokha komanso imene ikubwerayo. (aiōn )
cu mult mai presus de orice stăpânire, autoritate, putere, domnie și orice nume care se numește, nu numai în acest veac, ci și în cel ce va să vină. (aiōn )
mmene inu munkakhalamo pamene munkatsatira njira za dziko lapansi ndi za ulamuliro waufumu wa mlengalenga, mzimu umene ukugwira ntchito tsopano mwa amene samvera. (aiōn )
în care umblați odinioară, după cursul acestei lumi, după prințul puterii aerului, duhul care lucrează acum în copiii neascultătorilor. (aiōn )
ndi cholinga chakuti mʼnthawi imene ikubwera, Iyeyo adzaonetse chuma choposa cha chisomo chake, choonetsedwa mwa kukoma mtima kwake kwa ife mwa Khristu Yesu. (aiōn )
pentru ca în veacurile viitoare să arate bogăția nespus de mare a harului Său în bunătatea Sa față de noi în Hristos Isus; (aiōn )
Ndinasankhidwa kuti ndifotokoze momveka bwino kwa munthu aliyense za chinsinsi chimenechi, chinsinsi chimene kuyambira kale chinali chobisika mwa Mulungu amene analenga zinthu zonse. (aiōn )
și să fac pe toți oamenii să vadă care este administrarea misterului care de veacuri a fost ascuns în Dumnezeu, care a creat toate lucrurile prin Isus Hristos, (aiōn )
Chimenechi chinali chikonzero chamuyaya cha Mulungu, chimene chinachitika kudzera mwa Khristu Yesu Ambuye athu. (aiōn )
conform scopului veșnic pe care l-a împlinit în Hristos Isus, Domnul nostru. (aiōn )
Iyeyo akhale ndi ulemu mu mpingo ndi mwa Khristu Yesu pa mibado yonse mpaka muyaya. Ameni. (aiōn )
Lui să fie slava în adunare și în Hristos Isus, în toate generațiile, în vecii vecilor. Amin. (aiōn )
Pakuti sitikulimbana ndi thupi ndi magazi, koma tikulimbana ndi maufumu, maulamuliro, mphamvu za dziko la mdima, ndi mphamvu zoyipa kwambiri zauzimu zamlengalenga. (aiōn )
Căci lupta noastră nu este împotriva cărnii și a sângelui, ci împotriva principatelor, împotriva puterilor, împotriva stăpânitorilor lumii, a întunericului acestui veac și împotriva forțelor spirituale ale răutății din locurile cerești. (aiōn )
Kwa Mulungu ndi Atate athu, kukhale ulemerero mpaka muyaya. Ameni. (aiōn )
Acum, a Dumnezeului și Tatălui nostru să fie gloria în vecii vecilor! Amin. (aiōn )
chinsinsi chimene chakhala chikubisika kwa nthawi ndi mibado, koma tsopano chawululidwa kwa oyera mtima. (aiōn )
taina care a fost ascunsă de veacuri și de generații. Dar acum a fost descoperit sfinților Săi, (aiōn )
Adzalangidwa ndi chiwonongeko chamuyaya ndipo sadzaonanso nkhope ya Ambuye ndi ulemerero wamphamvu zake (aiōnios )
care va plăti pedeapsa: distrugerea veșnică de la fața Domnului și de la gloria puterii sale, (aiōnios )
Ambuye athu Yesu Khristu mwini ndi Mulungu Atate wathu, amene anatikonda ife ndipo mwachisomo chake anatipatsa kulimba mtima kwamuyaya ndi chiyembekezo chabwino, (aiōnios )
Iar Domnul nostru Iisus Hristos însuși și Dumnezeu Tatăl nostru, care ne-a iubit și ne-a dat prin har mângâierea veșnică și buna nădejde, (aiōnios )
Ndipo pa chifukwa chimenechi, Mulungu anandichitira chifundo, kuti mwa ine, wochimwitsitsa, Khristu Yesu aonetse kuleza mtima kwake konse kuti ndikhale chitsanzo cha omwe angathe kumukhulupirira ndi kulandira moyo wosatha. (aiōnios )
Totuși, din această cauză am obținut îndurare, pentru ca, în mine mai întâi, Isus Hristos să-și arate toată răbdarea ca exemplu pentru cei care urmau să creadă în el pentru viața veșnică. (aiōnios )
Tsopano kwa Mfumu yamuyaya, yosafa, yosaoneka, amene Iye yekha ndiye Mulungu, kukhale ulemu ndi ulemerero mpaka muyaya. Ameni. (aiōn )
Acum, Regelui veșnic, nemuritor și invizibil, lui Dumnezeu, care este singurul înțelept, să fie cinstea și gloria în vecii vecilor. Amin. (aiōn )
Menya nkhondo yabwino yachikhulupiriro. Gwiritsitsa moyo wosatha umene anakuyitanira pamene unavomereza bwino lomwe pamaso pa mboni zambiri. (aiōnios )
Luptă lupta cea bună a credinței. Apucă-te de viața veșnică la care ai fost chemat și ai mărturisit buna mărturisire în fața multor martori. (aiōnios )
Ndiye yekha wosafa ndipo amakhala mʼkuwala koopsa. Mulungu amene munthu aliyense sanamuone. Kwa Iye kukhale ulemu ndi mphamvu mpaka muyaya. Ameni. (aiōnios )
El singur are nemurirea, care locuiește într-o lumină de neatins, pe care nimeni nu l-a văzut și nici nu poate să-l vadă, căruia i se cuvine cinstea și puterea veșnică. Amin. (aiōnios )
Anthu onse amene ali ndi chuma uwalamule kuti asanyade kapena kuyika mitima yawo pa chuma chimene nʼchosadalirika. Koma chiyembekezo chawo chikhale mwa Mulungu amene amatipatsa mowolowamanja zonse zotisangalatsa. (aiōn )
Îndemnați-i pe cei ce sunt bogați în veacul acesta să nu se îngâmfe și să nu-și pună nădejdea în bogăția nesigură, ci în Dumnezeul cel viu, care ne dăruiește din belșug toate cele de care ne putem bucura; (aiōn )
Iye anatipulumutsa ndipo anatiyitanira ku moyo oyera mtima, osati chifukwa cha chilichonse chimene tinachita, koma chifukwa cha chikonzero ndi chisomo chake. Chisomo chimenechi anatipatsa ife mwa Khristu Yesu nthawi isanayambe. (aiōnios )
care ne-a salvat și ne-a chemat cu o chemare sfântă, nu după faptele noastre, ci după propriul său scop și har, care ne-a fost dat în Isus Hristos înainte de veșnicie, (aiōnios )
Choncho ndikupirira chilichonse chifukwa cha osankhidwa, kuti nawonso apulumutsidwe ndi Khristu Yesu ndi kulandira ulemerero wosatha. (aiōnios )
De aceea îndur toate lucrurile de dragul celor aleși, pentru ca și ei să dobândească mântuirea care este în Cristos Isus cu glorie veșnică. (aiōnios )
Paja Dema anandisiya chifukwa chokonda dziko lapansi lino, ndipo anapita ku Tesalonika. Kresike anapita ku Galatiya ndipo Tito anapita ku Dalimatiya. (aiōn )
căci Demas m-a părăsit, iubind lumea de acum, și s-a dus la Tesalonic, Crescens în Galatia și Tit în Dalmația. (aiōn )
Ambuye adzandilanditsa ku chilichonse chofuna kundichita choyipa ndipo adzandisamalira bwino mpaka kundilowetsa chonse mu ufumu wake wakumwamba. Kwa Iye kukhale ulemerero mpaka muyaya. (aiōn )
Și Domnul mă va izbăvi de orice lucrare rea și mă va păstra pentru Împărăția Sa cerească. A lui să fie gloria în vecii vecilor. Amin. (aiōn )
ndi kuwapatsa chiyembekezo cha moyo wosatha, umene Mulungu amene sanama, analonjeza nthawi isanayambe. (aiōnios )
în speranța vieții veșnice, pe care Dumnezeu, care nu poate minți, a făgăduit-o înainte de începutul veacurilor, (aiōnios )
Chisomo chimatiphunzitsa kukana moyo osalemekeza Mulungu komanso zilakolako za dziko lapansi. Ndipo chimatiphunzitsa kukhala moyo odziletsa, olungama ndi opembedza Mulungu nthawi ino, (aiōn )
instruindu-ne pentru ca, lepădându-ne de impietate și de poftele lumești, să trăim sobru, drept și evlavios în veacul acesta; (aiōn )
kuti titalungamitsidwa mwachisomo chake, tikhale olowamʼmalo okhala ndi chiyembekezo cha moyo wosatha. (aiōnios )
pentru ca, fiind îndreptățiți prin harul său, să fim făcuți moștenitori, potrivit cu speranța vieții veșnice. (aiōnios )
Mwina chifukwa chimene unasiyana naye kwa kanthawi ndi chakuti ukhale nayenso nthawi zonse. (aiōnios )
De aceea, poate că a fost despărțit de voi pentru o vreme, pentru ca voi să-l aveți pentru totdeauna, (aiōnios )
Koma masiku otsiriza ano, Mulungu wayankhula nafe kudzera mwa Mwana wake. Mwanayu anamusankha kuti akhale mwini wa zinthu zonse, ndiponso Mulungu analenga dziko lonse kudzera mwa Iye. (aiōn )
la sfârșitul acestor zile, ne-a vorbit prin Fiul Său, pe care L-a pus moștenitor al tuturor lucrurilor și prin care a făcut și lumile. (aiōn )
Koma za Mwana wake akuti, “Inu Mulungu, mpando wanu waufumu udzakhala mpaka muyaya, ndipo mudzaweruza molungama mu ufumu wanu. (aiōn )
Dar despre Fiul spune, “Tronul Tău, Dumnezeule, este în vecii vecilor. Sceptrul dreptății este sceptrul Împărăției Tale. (aiōn )
Ndipo penanso anati, “Iwe ndiwe wansembe mpaka muyaya, monga mwa unsembe wa Melikizedeki.” (aiōn )
După cum spune și în alt loc, “Ești preot pentru totdeauna, după ordinul lui Melchisedec.” (aiōn )
Atasanduka wangwiro kotheratu, anakhala gwero la chipulumutso chosatha kwa onse omvera Iye. (aiōnios )
Fiind desăvârșit, el a devenit pentru toți cei care îl ascultă autorul mântuirii veșnice, (aiōnios )
za maubatizo, za kusanjika manja, za kuuka kwa akufa ndi za chiweruzo chotsiriza. (aiōnios )
a învățăturii despre botezuri, despre punerea mâinilor, despre învierea morților și despre judecata veșnică. (aiōnios )
Analawa kukoma kwa mawu a Mulungu ndi mphamvu za nthawi ikubwera. (aiōn )
și au gustat cuvântul bun al lui Dumnezeu și puterile veacului viitor, (aiōn )
Yesu anatitsogolera kupita kumeneko, nalowako mʼmalo mwathu. Iye anasanduka Mkulu wa ansembe onse wamuyaya, monga mwa dongosolo la unsembe wa Melikizedeki. (aiōn )
unde, ca un precursor, Isus a intrat pentru noi, devenind Mare Preot pentru totdeauna, după rânduiala lui Melchisedec. (aiōn )
Pakuti Mulungu anamuchitira umboni kuti, “Iwe ndi wansembe wamuyaya, monga mwa dongosolo la unsembe wa Melikizedeki.” (aiōn )
căci este mărturisit, “Ești preot pentru totdeauna, conform ordinului lui Melchisedec.” (aiōn )
Koma Yesu ankakhala wansembe ndi lumbiro pamene Mulungu anati, “Ambuye analumbira ndipo sangasinthe maganizo ake, ‘Iwe ndi wansembe wamuyaya.’” (aiōn )
(căci, într-adevăr, au fost făcuți preoți fără jurământ), ci el cu jurământ, prin cel care spune despre el, “Domnul a jurat și nu se va răzgândi, 'Ești preot pentru totdeauna, conform ordinului lui Melchisedec.”” (aiōn )
Koma Yesu popeza ndi wamuyaya, unsembe wake ndi wosatha. (aiōn )
Dar el, pentru că trăiește veșnic, are o preoție neschimbată. (aiōn )
Pakuti lamulo limasankha anthu amene ndi ofowoka kukhala akulu a ansembe; koma lumbiro, lomwe linabwera pambuyo pa lamulo, linasankha Mwana, amene anapangidwa kukhala wangwiro kwamuyaya. (aiōn )
Căci legea numește ca mari preoți pe oameni care au slăbiciuni, dar cuvântul jurământului, care a venit după lege, numește pentru totdeauna un Fiu care a fost desăvârșit. (aiōn )
Iye sanalowemo ndi magazi ambuzi yayimuna, ana angʼombe amphongo, koma analowa Malo Opatulika kamodzi kokha ndi magazi ake, atatikonzera chipulumutso chosatha. (aiōnios )
și nici prin sângele țapilor și vițeilor, ci prin propriul sânge, a intrat o dată pentru totdeauna în Locul Sfânt, obținând răscumpărarea veșnică. (aiōnios )
nʼkoposa kotani magazi a Khristu, amene mwa Mzimu wamuyaya anadzipereka yekha kwa Mulungu kukhala nsembe yopanda chilema. Iye adzayeretsa chikumbumtima chathu pochotsa ntchito za imfa, kuti ife titumikire Mulungu wamoyo. (aiōnios )
cu cât mai mult sângele lui Cristos, care, prin Duhul etern, s-a oferit pe sine însuși fără cusur lui Dumnezeu, va curăța conștiința voastră de fapte moarte pentru a sluji Dumnezeului viu? (aiōnios )
Pa chifukwa chimenechi Khristu ndi mʼkhalapakati wa pangano latsopano, kuti iwo amene anayitanidwa alandire chuma chamuyaya, pakuti Iye tsopano anafa ngati dipo lomasula iwo ku machimo amene anachita ali pansi pa pangano loyamba lija. (aiōnios )
De aceea, el este mijlocitorul unui nou legământ, întrucât a avut loc o moarte pentru răscumpărarea fărădelegilor care au fost sub primul legământ, pentru ca cei care au fost chemați să primească promisiunea moștenirii veșnice. (aiōnios )
Zikanatero bwenzi Khristu atamva zowawa kambirimbiri chilengedwere cha dziko lapansi. Koma tsopano anaoneka kamodzi kokha chifukwa cha onse pa nthawi yotsiriza kuti achotse tchimo podzipereka yekha nsembe. (aiōn )
altfel trebuie să fi suferit adeseori de la întemeierea lumii. Dar acum, o singură dată, la sfârșitul veacurilor, el s-a arătat pentru a înlătura păcatul prin jertfa lui însuși. (aiōn )
Ndi chikhulupiriro timazindikira kuti dziko lapansi ndi la mmwamba zinapangidwa ndi Mawu a Mulungu, ndikuti zinthu zoonekazi zinachokera ku zinthu zosaoneka. (aiōn )
Prin credință înțelegem că universul a fost alcătuit prin Cuvântul lui Dumnezeu, astfel încât ceea ce se vede nu a fost făcut din lucruri vizibile. (aiōn )
Yesu Khristu ndi yemweyo dzulo, lero ndi kunthawi zonse. (aiōn )
Isus Hristos este același ieri, astăzi și în veci. (aiōn )
Mulungu wamtendere, amene kudzera mʼmagazi a pangano lamuyaya anaukitsa Ambuye athu Yesu kwa akufa, amene ndi Mʼbusa wamkulu, (aiōnios )
Și Dumnezeul păcii, care a înviat din morți pe marele păstor al oilor cu sângele unui legământ veșnic, pe Domnul nostru Isus, (aiōnios )
akupatseni chilichonse chabwino kuti muchite chifuniro chake ndipo Mulungu achite mwa ife, chimene chingamukomere kudzera mwa Yesu Khristu. Kwa Iye kukhale ulemerero ku nthawi zanthawi, Ameni. (aiōn )
să vă facă desăvârșiți în orice lucrare bună, ca să faceți voia Lui, lucrând în voi ceea ce este plăcut înaintea Lui, prin Isus Hristos, căruia I se cuvine slava în vecii vecilor. Amin. (aiōn )
Lilime nalonso ndi moto, dziko la zoyipa pakati pa ziwalo za thupi. Limawononga munthu yense wathunthu. Limayika zonse za moyo wake pa moto, ndipo moto wake ndi wochokera ku gehena. (Geenna )
Și limba este un foc. Lumea nelegiuirii dintre mădularele noastre este limba, care spurcă tot trupul și dă foc cursului firii, și este incendiată de Gheenă. (Geenna )
Popeza mwabadwanso, osati ndi mbewu imene imawonongeka, koma imene siwonongeka, ndiye kuti ndi Mawu a Mulungu amoyo ndi okhalitsa. (aiōn )
fiind născuți din nou, nu din sămânță coruptibilă, ci din incoruptibilă, prin cuvântul lui Dumnezeu, care trăiește și rămâne în veci. (aiōn )
koma mawu a Ambuye adzakhala mpaka muyaya.” Ndipo awa ndi mawu amene tinalalikira kwa inu. (aiōn )
dar cuvântul Domnului este veșnic.” Acesta este cuvântul de Buna Vestire care v-a fost propovăduit. (aiōn )
Ngati wina ayankhula, ayankhuledi mawu enieni a Mulungu. Ngati wina atumikira, atumikire ndi mphamvu imene Mulungu amapereka, kuti pa zonse Mulungu alemekezedwe mwa Yesu Khristu. Kwa Iye kukhale ulemerero ndi mphamvu mpaka muyaya, Ameni. (aiōn )
Dacă cineva vorbește, să fie ca și cum ar fi chiar cuvintele lui Dumnezeu. Dacă cineva slujește, să fie ca din puterea pe care o dă Dumnezeu, pentru ca în toate lucrurile să fie glorificat Dumnezeu prin Isus Hristos, căruia îi aparțin gloria și stăpânirea în vecii vecilor. Amin. (aiōn )
Ndipo Mulungu wachisomo chonse, amene anakuyitanani ku ulemerero wake wamuyaya mwa Khristu, mutamva zowawa pa kanthawi, adzakukonzaninso ndi kukulimbitsani pa maziko olimba. (aiōnios )
Dar fie ca Dumnezeul oricărui har, care v-a chemat la gloria Sa eternă prin Hristos Isus, după ce ați suferit puțin, să vă desăvârșească, să vă întărească, să vă întărească și să vă așeze. (aiōnios )
Kwa Iye kukhale mphamvu mpaka muyaya, Ameni. (aiōn )
A lui să fie gloria și puterea în vecii vecilor. Amin. (aiōn )
Mudzalandiridwa bwino kwambiri mu ufumu wosatha wa Ambuye ndi Mpulumutsi wathu Yesu Khristu. (aiōnios )
Căci astfel veți avea din belșug intrarea în Împărăția veșnică a Domnului și Mântuitorului nostru, Isus Hristos. (aiōnios )
Pakuti Mulungu sanalekerere angelo atachimwa paja, koma anawaponya mʼndende, nawayika mʼmaenje amdima, kuwasunga kuti adzaweruzidwe. (Tartaroō )
Căci, dacă Dumnezeu nu a cruțat pe îngeri când au păcătuit, ci i-a aruncat în Tartar și i-a trimis în gropile întunericului, ca să fie rezervați pentru judecată; (Tartaroō )
Koma kulani mu chisomo ndi mʼchidziwitso cha Ambuye ndi Mpulumutsi wathu Yesu Khristu. Kwa Iye kukhale ulemerero tsopano mpaka muyaya. Ameni. (aiōn )
Ci creșteți în harul și în cunoașterea Domnului și Mântuitorului nostru Isus Hristos. A lui să fie gloria acum și în veci. Amin. (aiōn )
Moyowo unaoneka, tinawuona ndipo tikuchitira umboni. Tikukulalikirani za moyo wosatha umene unali ndi Atate ndipo unaonekera kwa ife. (aiōnios )
(și viața a fost descoperită, și noi am văzut, și mărturisim și vă vestim viața, viața veșnică, care era la Tatăl și care ne-a fost descoperită); (aiōnios )
Dziko lapansi likupita pamodzi ndi zilakolako zake, koma amene amachita chifuniro cha Mulungu amakhalapo mpaka muyaya. (aiōn )
Lumea trece cu poftele ei, dar cel care face voia lui Dumnezeu rămâne pentru totdeauna. (aiōn )
Ndipo chimene anatilonjeza nʼchimenechi: moyo wosatha. (aiōnios )
Aceasta este făgăduința pe care ne-a promis-o: viața veșnică. (aiōnios )
Aliyense amene amadana ndi mʼbale wake ndi wakupha, ndipo inu mukudziwa kuti wopha anthu mwa iye mulibe moyo wosatha. (aiōnios )
Oricine își urăște fratele este un ucigaș, și știți că niciun ucigaș nu are viață veșnică rămasă în el. (aiōnios )
Ndipo umboniwo ndi uwu: Mulungu anatipatsa moyo wosatha, ndipo moyowu uli mwa Mwana wake. (aiōnios )
Mărturia este aceasta: Dumnezeu ne-a dat viața veșnică, iar această viață este în Fiul său. (aiōnios )
Ine ndikulemba zimenezi kwa inu, amene mwakhulupirira dzina la Mwana wa Mulungu kuti mudziwe kuti muli ndi moyo wosatha. (aiōnios )
Am scris aceste lucruri pentru voi, care credeți în Numele Fiului lui Dumnezeu, ca să știți că aveți viața veșnică și să credeți în continuare în Numele Fiului lui Dumnezeu. (aiōnios )
Tikudziwa kuti Mwana wa Mulungu anafika ndipo anatipatsa nzeru, kuti timudziwe Iye amene ali woona. Ndipo ife tili mwa Iye amene ndi woona, Mwana wake, Yesu Khristu. Iye ndi Mulungu woona ndi moyo wosatha. (aiōnios )
Știm că Fiul lui Dumnezeu a venit și ne-a dat pricepere, ca să cunoaștem pe cel adevărat; și noi suntem în cel adevărat, în Fiul său Isus Hristos. Acesta este adevăratul Dumnezeu și viața veșnică. (aiōnios )
Timakukondani chifukwa cha choonadi chimene chimakhala mwa ife ndipo chidzakhala mwa ife mpaka muyaya. (aiōn )
pentru adevărul care rămâne în noi și care va fi cu noi în veci: (aiōn )
Ndipo mukumbukire angelo amene sanakhutire ndi maudindo awo, koma anasiya malo awo. Angelo amenewa Mulungu anawamanga ndi maunyolo osatha, ndipo akuwasunga mʼmalo a mdima mpaka tsiku lalikulu lachiweruzo. (aïdios )
Pe îngerii care nu și-au păstrat primul domeniu, ci și-au părăsit propria locuință, i-a ținut în legături veșnice, sub întuneric, pentru judecata din ziua cea mare. (aïdios )
Musayiwale mizinda ya Sodomu ndi Gomora ija, ndi mizinda yoyandikana nayo. Anthu mʼmenemo anadziperekanso kuchita zadama ndi kuchita zonyansa zachilendo. Mizinda imeneyi yakhala ngati chitsanzo cha amene adzalangidwa ndi moto wosatha. (aiōnios )
La fel ca Sodoma și Gomora și orașele din jurul lor, care, la fel ca acestea, s-au dedat la imoralitate sexuală și au umblat după trupuri străine, sunt arătate ca exemplu, suferind pedeapsa focului veșnic. (aiōnios )
Iwowa ali ngati mafunde awukali apanyanja, amene amatulutsa thovu la zonyansa zawo. Amenewa ali ngati nyenyezi zosochera, ndipo Mulungu akuwasungira mdima wandiweyani mpaka muyaya. (aiōn )
valuri sălbatice ale mării, care își scot spuma rușinii lor; stele rătăcitoare, cărora le-a fost rezervată pentru totdeauna negura întunericului. (aiōn )
Khalani mʼchikondi cha Mulungu pamene mukudikira chifundo cha Ambuye athu Yesu Khristu kuti akubweretsereni moyo wosatha. (aiōnios )
Păstrați-vă în dragostea lui Dumnezeu, așteptând îndurarea Domnului nostru Isus Hristos pentru viața veșnică. (aiōnios )
kwa Mulungu yekhayo, Mpulumutsi wathu, kwa Iye kukhale ulemerero, ukulu, mphamvu ndi ulamuliro, mwa Yesu Khristu Ambuye athu, kuyambira isanayambe nthawi, tsopano mpaka muyaya. Ameni. (aiōn )
lui Dumnezeu, Mântuitorul nostru, singurul înțelept, fie slava și maiestatea, stăpânirea și puterea, acum și pururea și în vecii vecilor. Amin. (aiōn )
ndipo watisandutsa mafumu ndi ansembe kuti tizitumikira Mulungu ndi Atate ake. Kwa Iye kukhale ulemerero ndi mphamvu ku nthawi zosatha, Ameni. (aiōn )
și ne-a făcut să fim un regat, preoți ai Dumnezeului și Tatălui său — lui să fie gloria și stăpânirea în vecii vecilor. Amin. (aiōn )
Ine ndine Wamoyo; ndinali wakufa ndipo taona ndine wamoyo mpaka muyaya! Ndipo ndili ndi makiyi a imfa ndi Hade. (aiōn , Hadēs )
și Cel viu. Am fost mort și iată că sunt viu în vecii vecilor. Amin. Eu am cheile Morții și ale Hadesului. (aiōn , Hadēs )
Nthawi zonse zamoyozo zimapereka ulemerero, ulemu ndi mayamiko kwa uja wokhala pa mpando waufumu, amene ali ndi moyo wamuyaya. (aiōn )
Când făpturile vii vor da slavă, cinste și mulțumire Celui ce șade pe tron, Celui ce trăiește în vecii vecilor, (aiōn )
Izi zikamachitika akuluakulu 24 aja amadzigwetsa pansi pamaso pa wokhala pa mpando waufumuyo, namupembedza wokhala ndi moyo wamuyayayo. Iwo amaponya pansi zipewa zawo zaufumu patsogolo pa mpando waufumu nati: (aiōn )
cei douăzeci și patru de bătrâni se vor arunca înaintea Celui ce șade pe tron și se vor închina Celui ce trăiește în vecii vecilor și își vor arunca coroanele înaintea tronului, zicând: (aiōn )
Kenaka ndinamva mawu a cholengedwa chilichonse kumwamba, pa dziko lapansi, kunsi kwa dziko lapansi, pa nyanja ndi zonse zili mʼmenemo zikuyimba kuti, “Kwa wokhala pa mpando waufumu ndi kwa Mwana Wankhosa, kukhale mayamiko, ulemu, ulemerero ndi mphamvu (aiōn )
Și am auzit toate făpturile care sunt în ceruri, pe pământ, sub pământ, pe mare și tot ce este în ele, zicând: “Binecuvântarea, cinstea, slava și stăpânirea să fie pentru Cel ce șade pe scaunul de domnie și pentru Miel, în vecii vecilor! Amin!” (aiōn )
Nditayangʼana patsogolo panga ndinaona kavalo wotuwa! Wokwerapo wake dzina lake linali Imfa ndipo Hade inali kumutsatira pambuyo pake. Anapatsidwa ulamuliro pa gawo limodzi la magawo anayi a dziko lapansi kuti aphe ndi lupanga, njala, mliri, ndi zirombo zakuthengo za mʼdziko lapansi. (Hadēs )
Și iată un cal palid, iar numele celui care ședea pe el era Moartea. Hades îl urma cu el. I s-a dat autoritate asupra unui sfert din pământ, ca să ucidă cu sabia, cu foametea, cu moartea și cu animalele sălbatice de pe pământ. (Hadēs )
Iwo anati, “Ameni! Matamando ndi ulemerero, nzeru, mayamiko, ulemu, ulamuliro ndi mphamvu zikhale kwa Mulungu wathu kunthawi zanthawi, Ameni!” (aiōn )
zicând: “Amin! Binecuvântare, glorie, înțelepciune, mulțumire, onoare, putere și tărie să fie pentru Dumnezeul nostru în vecii vecilor! Amin.” (aiōn )
Mngelo wachisanu anayimba lipenga lake, ndipo ndinaona nyenyezi ikugwa pa dziko lapansi kuchokera ku thambo. Nyenyeziyo inapatsidwa kiyi ya ku chidzenje chakuya. (Abyssos )
Îngerul al cincilea a sunat din glas și am văzut din cer o stea care a căzut pe pământ. Cheia de la groapa abisului i-a fost dată. (Abyssos )
Nyenyeziyo itatsekula pa chidzenje chakuyacho panatuluka utsi ngati wochokera mʼngʼanjo yayikulu. Dzuwa ndi thambo zinada chifukwa cha utsi ochokera mʼdzenjemo. (Abyssos )
El a deschis groapa abisului și din groapă a ieșit fum ca fumul unui cuptor aprins. Soarele și aerul s-au întunecat din cauza fumului care ieșea din groapă. (Abyssos )
Mfumu yawo inali mngelo wolamulira Chidzenje chakuya chija. Mʼchihebri dzina lake ndi Abadoni ndipo mʼChigriki ndi Apoliyoni (tanthauzo lake ndiye kuti, Wowononga). (Abyssos )
Ei au peste ei ca rege pe îngerul abisului. Numele lui în ebraică este “Abaddon”, dar în greacă are numele “Apollyon”. (Abyssos )
Mngeloyo analumbira mʼdzina la Iye wokhala ndi moyo mpaka muyaya, amene analenga kumwamba ndi zonse zili kumeneko, dziko lapansi ndi zonse zili mʼmenemo, nyanja ndi zonse zili mʼmenemo, nati, “Pasakhalenso zochedwa tsopano! (aiōn )
și a jurat pe Cel ce trăiește în vecii vecilor, care a creat cerul și lucrurile care sunt în el, pământul și lucrurile care sunt în el, marea și lucrurile care sunt în ea, că nu va mai fi nici o întârziere, (aiōn )
Tsono zikadzatsiriza umboni wawowo, chirombo chotuluka mʼChidzenje chakuya chija chidzachita nawo nkhondo nʼkuzigonjetsa mpaka kuzipha. (Abyssos )
După ce-și vor fi isprăvit mărturia lor, fiara care se va ridica din prăpastie va face război cu ei, îi va birui și-i va ucide. (Abyssos )
Mngelo wachisanu ndi chiwiri anawomba lipenga lake, ndipo kumwamba kunamveka mawu ofuwula amene anati, “Ufumu wa dziko lapansi uli mʼmanja mwa Ambuye athu ndi Khristu wake uja, ndipo adzalamulira mpaka muyaya.” (aiōn )
Îngerul al șaptelea a sunat și au urmat glasuri mari în ceruri, care ziceau: “Împărăția lumii a devenit Împărăția Domnului nostru și a Hristosului Său. El va domni în vecii vecilor!” (aiōn )
Kenaka ndinaona mngelo wina akuwuluka mu mlengalenga ndipo anali ndi Uthenga Wabwino wamuyaya woti akalalikire kwa anthu okhala pa dziko lapansi, kwa a mtundu uliwonse, a fuko lililonse, a chiyankhulo chilichonse ndi kwa anthu onse. (aiōnios )
Și am văzut un înger care zbura din mijlocul cerului și care avea o veste veșnică, pe care trebuia să o vestească celor ce locuiesc pe pământ, oricărui neam, seminție, limbă și popor. (aiōnios )
Ndipo utsi wa moto wowazunzawo udzakwera kumwamba mpaka muyaya. Sikudzakhala kupumula usana ndi usiku kwa amene anapembedza chirombo chija ndi fano lake kapena kwa aliyense amene analembedwa chizindikiro cha dzina lake lija.” (aiōn )
Fumul chinului lor se va ridica în vecii vecilor. Nu au odihnă zi și noapte, cei care se închină fiarei și chipului ei și oricine primește semnul numelui ei. (aiōn )
Ndipo kenaka chimodzi cha zamoyo zinayi zija chinapereka kwa angelo asanu ndi awiri mbale zisanu ndi ziwiri zodzaza ndi ukali wa Mulungu amene ali ndi moyo mpaka muyaya. (aiōn )
Una din cele patru făpturi vii a dat celor șapte îngeri șapte cupe de aur pline cu mânia lui Dumnezeu, care trăiește în vecii vecilor. (aiōn )
Chirombo chimene wachionachi chinalipo kale koma tsopano kulibe ndipo chidzatuluka ku chidzenje chakuya ndi kupita kukawonongedwa. Anthu okhala pa dziko lapansi amene mayina awo sanalembedwe mʼbuku lamoyo kuyambira pa kulengedwa kwa dziko lapansi adzadabwa pamene adzaona chirombocho, chifukwa chinalipo kale, tsopano kulibe, komabe chidzabwera. (Abyssos )
Fiara pe care ai văzut-o a fost și nu mai este; și este pe cale să iasă din abis și să meargă la pieire. Cei care locuiesc pe pământ și ale căror nume nu au fost scrise în cartea vieții de la întemeierea lumii se vor minuna când vor vedea că fiara a fost și nu este, și va fi prezentă. (Abyssos )
Ndipo anafuwulanso kuti, “Haleluya! Utsi wochokera kwa mkazi wadamayo udzakwera kumwamba mpaka muyaya.” (aiōn )
Al doilea a zis: “Aleluia! Fumul ei se ridică în vecii vecilor”. (aiōn )
Koma chirombocho chinagwidwa pamodzi ndi mneneri wonyenga uja amene anachita zizindikiro zodabwitsa pamaso pake. Ndi zizindikirozi anasocheretsa amene analembedwa chizindikiro cha chirombocho napembedza fano lake. Onse awiri anaponyedwa amoyo mʼnyanja yamoto yasulufule wotentha. (Limnē Pyr )
Fiara a fost prinsă și, împreună cu ea, falsul profet care făcea semnele pe care le făcea în fața lui, prin care îi înșela pe cei care primiseră semnul fiarei și pe cei care se închinau chipului ei. Aceștia doi au fost aruncați de vii în lacul de foc care arde cu sulf. (Limnē Pyr )
Ndipo ndinaona mngelo akutsika kuchokera kumwamba ali ndi kiyi ya ku chidzenje chakuya chija atanyamula mʼdzanja lake unyolo waukulu. (Abyssos )
Am văzut un înger coborând din cer, având în mână cheia prăpastiei și un lanț mare. (Abyssos )
Anamuponya ku chidzenje chakuya chija namutsekera ndi kiyi ndi kumatirira pa khomopo kuti asatulukenso kukanyenga mitundu ya anthu mpaka patapita zaka 1,000. Zikadzatha zakazo, adzamumasula kwa kanthawi pangʼono chabe. (Abyssos )
l-a aruncat în abis, l-a închis și l-a pecetluit peste el, ca să nu mai înșele neamurile până la sfârșitul celor o mie de ani. După aceasta, el trebuie să fie eliberat pentru o scurtă perioadă de timp. (Abyssos )
Ndipo Mdierekezi amene anawanyenga, anaponyedwa mʼnyanja ya sulufule wotentha, kumene kunaponyedwa chirombo chija ndi mneneri wonama uja. Iwo adzazunzika usiku ndi usana kwamuyaya. (aiōn , Limnē Pyr )
Diavolul care i-a înșelat a fost aruncat în iazul de foc și de sulf, unde sunt și fiara și falsul profet. Ei vor fi chinuiți zi și noapte în vecii vecilor. (aiōn , Limnē Pyr )
Nyanja inapereka amene anaferamo ndipo imfa ndi Hade zinapereka akufa ake ndipo munthu aliyense anaweruzidwa monga mwa ntchito zake. (Hadēs )
Marea a dat pe față morții care se aflau în ea. Moartea și Hadesul au renunțat la morții care erau în ele. Au fost judecați, fiecare după faptele sale. (Hadēs )
Kenaka imfa ndi Hade zinaponyedwa mʼnyanja ya moto. Nyanja yamoto ndiyo imfa yachiwiri. (Hadēs , Limnē Pyr )
Moartea și Hadesul au fost aruncate în lacul de foc. Aceasta este a doua moarte, lacul de foc. (Hadēs , Limnē Pyr )
Ngati dzina la wina aliyense silinapezeke mʼBuku Lamoyo, anaponyedwa mʼnyanja yamoto. (Limnē Pyr )
Dacă cineva nu era găsit scris în cartea vieții, era aruncat în lacul de foc. (Limnē Pyr )
Koma amantha, osakhulupirira, okonda zonyansa, opha anthu, achiwerewere, amatsenga, opembedza mafano ndi abodza, malo awo adzakhala nyanja yamoto ya sulufule wotentha. Iyi ndi imfa yachiwiri.” (Limnē Pyr )
Dar pentru cei lași, necredincioși, păcătoși, abominabili, ucigași, imorali, vrăjitori, închinători la idoli și toți mincinoșii, partea lor este în lacul care arde cu foc și sulf, care este moartea a doua.” (Limnē Pyr )
Sipadzakhalanso usiku. Sadzafuna kuwala kwa nyale kapena kwa dzuwa pakuti Ambuye Mulungu adzakhala kuwala kwawo. Ndipo adzalamulira kwamuyaya. (aiōn )
Nu va mai fi noapte și nu vor avea nevoie de lumina lămpii sau de lumina soarelui, pentru că Domnul Dumnezeu îi va lumina. Ei vor domni în vecii vecilor. (aiōn )