Aionian Verses

Ngakhale kuti ana ake onse aamuna ndi aakazi anasonkhana kudzamutonthoza, iye anakana kutonthozedwa. Iye anati, “Ayi. Ndidzalira mpaka ndidzapite kwa mwana wanga ku manda.” Choncho Israeli anapitirirabe kulira mwana wake. (Sheol h7585)
(parallel missing)
Koma Yakobo anati, “Mwana wanga sapita nanu kumeneko; mkulu wake anamwalira ndipo watsala yekha. Ngati choyipa chitamuchitikira pa ulendo mukupitawu, ndiye kuti ndi mmene ndakalambiramu inu mudzandipha ndi chisoni chotere.” (Sheol h7585)
(parallel missing)
Tsopano mukanditengeranso uyu, nakaphedwa mu njira ndiye kuti mudzandikankhira ku manda ndi chisoni.’ (Sheol h7585)
(parallel missing)
ndipo akakaona kuti mnyamatayu palibe, basi akafa. Ife tidzakhala ngati takankhira abambo athu ku manda ndi chisoni. (Sheol h7585)
(parallel missing)
Koma Yehova akachita china chake chachilendo, nthaka nitsekula pakamwa pake ndi kuwameza iwo pamodzi ndi zonse zimene ali nazo, iwowa nʼkulowa mʼmanda ali moyo, pamenepo mudzazindikira kuti anthu amenewa ananyoza Yehova.” (Sheol h7585)
(parallel missing)
Analowa mʼmanda amoyo pamodzi ndi zonse zimene anali nazo. Nthaka inawatsekera ndi kuwawononga ndipo sanaonekenso. (Sheol h7585)
(parallel missing)
Pakuti mkwiyo wanga wayaka ngati moto, umene umayaka mpaka ku dziko la anthu akufa. Motowo udzanyeketsa dziko lapansi ndi zokolola zake ndipo udzapsereza maziko a mapiri. (Sheol h7585)
(parallel missing)
“Yehova amabweretsa imfa ndipo amaperekanso moyo, amatsitsira ku manda ndipo amawatulutsakonso. (Sheol h7585)
(parallel missing)
Anandimanga ndi zingwe za ku manda; misampha ya imfa inalimbana nane. (Sheol h7585)
(parallel missing)
Iwe uchite kwa iye molingana ndi nzeru zako, koma usalole kuti afe ndi ukalamba ndi kupita ku manda mwamtendere. (Sheol h7585)
(parallel missing)
Koma tsopano usamuyese ngati munthu wosalakwa. Iwe ndiwe munthu wanzeru. Udzadziwa choti uchite naye. Ngakhale ndi wokalamba, aphedwe ndithu.” (Sheol h7585)
(parallel missing)
Monga mtambo umazimirira ndi kukanganuka, momwemonso munthu amene walowa mʼmanda sabwerera. (Sheol h7585)
(parallel missing)
Zili kutali kupambana mayiko akumwamba, nanga ungachite chiyani? Ndi zakuya kupambana kuya kwa manda, nanga ungadziwe chiyani? (Sheol h7585)
(parallel missing)
“Aa, Inu mukanangondibisa mʼmanda ndi kundiphimba kuti ndisaoneke mpaka mkwiyo wanu utapita! Achikhala munandiyikira nthawi, kuti pambuyo pake mundikumbukirenso. (Sheol h7585)
(parallel missing)
Ngati nyumba imene ndikuyiyembekezera ndi manda, ngati ndiyala bedi langa mu mdima, (Sheol h7585)
(parallel missing)
Ndithu sindidzakhalanso ndi chiyembekezo chilichonse, polowa mʼmanda, pamene ndidzatsikira ku fumbi.” (Sheol h7585)
(parallel missing)
Zaka zawo zimatha ali mu ulemerero ndipo amatsikira ku manda mwamtendere. (Sheol h7585)
(parallel missing)
Monga momwe kutentha ndi chilala zimasungunulira madzi owundana ndi momwemonso mmene manda amachotsera omwe achimwa. (Sheol h7585)
(parallel missing)
Dziko la anthu akufa ndi lapululu pamaso pa Mulungu; chiwonongeko ndi chosaphimbidwa. (Sheol h7585)
(parallel missing)
Palibe amene amakukumbukirani pamene wamwalira; Amakutamandani ndani ali ku manda? (Sheol h7585)
(parallel missing)
Oyipa amabwerera ku manda, mitundu yonse imene imayiwala Mulungu. (Sheol h7585)
(parallel missing)
chifukwa Inu simudzandisiya ku manda, simudzalola kuti woyera wanu avunde. (Sheol h7585)
(parallel missing)
Anandimanga ndi zingwe za ku manda; misampha ya imfa inalimbana nane. (Sheol h7585)
(parallel missing)
Inu Yehova, munanditulutsa ku manda, munandisunga kuti ndisatsalire mʼdzenje. (Sheol h7585)
(parallel missing)
Yehova musalole kuti ndichite manyazi, pakuti ndalirira kwa Inu; koma oyipa achititsidwe manyazi ndipo agone chete mʼmanda. (Sheol h7585)
(parallel missing)
Monga nkhosa iwo ayenera kupita ku manda, ndipo imfa idzawadya. Olungama adzawalamulira mmawa; matupi awo adzavunda mʼmanda, kutali ndi nyumba zawo zaufumu. (Sheol h7585)
(parallel missing)
Koma Mulungu adzawombola moyo wanga kuchoka ku manda; ndithu Iye adzanditengera kwa Iye mwini. (Sheol h7585)
(parallel missing)
Mulole imfa itenge adani anga mwadzidzidzi; alowe mʼmanda ali amoyo pakuti choyipa chili pakati pawo. (Sheol h7585)
(parallel missing)
Pakuti chikondi chanu nʼchachikulu kwa ine; mwandipulumutsa ku malo ozama a manda. (Sheol h7585)
(parallel missing)
Pakuti ndili ndi mavuto ambiri ndipo moyo wanga ukuyandikira ku manda. (Sheol h7585)
(parallel missing)
Kodi ndi munthu uti angakhale ndi moyo ndi kusaona imfa? Kapena kudzipulumutsa yekha ku mphamvu ya manda? (Sela) (Sheol h7585)
(parallel missing)
Zingwe za imfa zinandizinga, zoopsa za ku dziko la anthu akufa zinandigwera; ndinapeza mavuto ndi chisoni. (Sheol h7585)
(parallel missing)
Ndikakwera kumwamba, Inu muli komweko; ndikakagona ku malo a anthu akufa, Inu muli komweko. (Sheol h7585)
(parallel missing)
Iwo adzati, “Monga momwe nkhuni zimamwazikira akaziwaza, ndi momwenso mafupa athu amwazikira pa khomo la manda.” (Sheol h7585)
(parallel missing)
tiwameze amoyo ngati manda, ndi athunthu ngati anthu otsikira mʼdzenje. (Sheol h7585)
(parallel missing)
Mapazi ake amatsikira ku imfa; akamayenda ndiye kuti akupita ku manda. (Sheol h7585)
(parallel missing)
Nyumba yake ndi njira yopita ku manda, yotsikira ku malo a anthu akufa. (Sheol h7585)
(parallel missing)
Koma amunawo sadziwa kuti akufa ali kale komweko, ndi kuti alendo ake alowa kale mʼmanda akuya. (Sheol h7585)
(parallel missing)
Manda ndi chiwonongeko ndi zosabisika pamaso pa Yehova, nanji mitima ya anthu! (Sheol h7585)
(parallel missing)
Munthu wanzeru amatsata njira yopita ku moyo kuti apewe malo okhala anthu akufa. (Sheol h7585)
(parallel missing)
Ukamukwapula ndi tsatsa udzapulumutsa moyo wake. (Sheol h7585)
(parallel missing)
Manda sakhuta, nawonso maso a munthu sakhuta. (Sheol h7585)
(parallel missing)
Manda, mkazi wosabala, nthaka yosakhuta madzi ndiponso moto womangoyakirayakira!” (Sheol h7585)
(parallel missing)
Ntchito iliyonse imene ukuyigwira, uyigwire ndi mphamvu zako zonse, pakuti ku manda kumene ukupita kulibe kugwira ntchito, kulibe malingaliro, chidziwitso ndiponso nzeru. (Sheol h7585)
(parallel missing)
Undiyike pamtima pako ngati chidindo, ngati chidindo cha pa dzanja lako; pakuti chikondi nʼchamphamvu ngati imfa, nsanje ndiyaliwuma ngati manda. Chikondi chimachita kuti lawilawi ngati malawi a moto wamphamvu. (Sheol h7585)
(parallel missing)
Nʼchifukwa chake ku manda sikukhuta ndipo kwayasama kwambiri kukamwa kwake; mʼmandamo mudzagweranso anthu otchuka a mu Yerusalemu pamodzi ndi anthu wamba ochuluka; adzagweramo ali wowowo, nʼkuledzera kwawoko. (Sheol h7585)
(parallel missing)
“Pempha chizindikiro kwa Yehova Mulungu wako, chikhale chozama ngati manda kapena chachitali ngati mlengalenga.” (Sheol h7585)
(parallel missing)
Ku manda kwatekeseka kuti akulandire ukamabwera; mizimu ya anthu akufa, aja amene anali atsogoleri a dziko lapansi, yadzutsidwa. Onse amene anali mafumu a mitundu ya anthu ayimiritsidwa pa mipando yawo. (Sheol h7585)
(parallel missing)
Ulemerero wako wonse walowa mʼmanda, pamodzi ndi nyimbo za azeze ako; mphutsi zayalana pogona pako ndipo chofunda chako ndi nyongolotsi. (Sheol h7585)
(parallel missing)
Koma watsitsidwa mʼmanda pansi penipeni pa dzenje. (Sheol h7585)
(parallel missing)
Inu mumayankhula monyada kuti, “Ife tinachita pangano ndi imfa, ife tachita mgwirizano ndi manda. Pamene mliri woopsa ukadzafika sudzatikhudza ife, chifukwa timadalira bodza ngati pothawirapo pathu ndi chinyengo ngati malo anthu obisalapo.” (Sheol h7585)
(parallel missing)
Pangano limene munachita ndi imfa lidzathetsedwa; mgwirizano wanu ndi manda udzachotsedwa. Pakuti mliri woopsa udzafika, ndipo udzakugonjetsani. (Sheol h7585)
(parallel missing)
Ine ndinaganiza kuti ndidzapita ku dziko la akufa pamene moyo ukukoma. (Sheol h7585)
(parallel missing)
Pakuti akumanda sangathe kukutamandani, akufa sangayimbe nyimbo yokutamandani. Iwo amene akutsikira ku dzenje sangakukhulupirireni. (Sheol h7585)
(parallel missing)
Mumapita kukapembedza fano la Moleki mutatenga mafuta ndi zonunkhira zochuluka. Munachita kutumiza akazembe anu kutali; inu ngakhale munapita ku manda kwenikweniko! (Sheol h7585)
(parallel missing)
“‘Ine Ambuye Yehova ndikuti: Pa nthawi imene mkungudzawo unatsikira ku manda, ndinawuza nyanja kuti iwulire maliro pakuwuphimba. Ndinawumitsa mitsinje ndipo madzi ambiri anaphwa. Ndinabweretsa mdima pa Lebanoni chifukwa cha mtengowo ndipo mitengo yonse ya mʼdzikomo inawuma. (Sheol h7585)
(parallel missing)
Mitundu ya anthu inagwedezeka pakumva mkokomo wa kugwa kwake, pamene ndinawutsitsira ku manda pamodzi ndi iwo amene anafa. Pamenepo ku dziko la akufa mitengo yonse ya ku Edeni pamodzi ndi ya ku Lebanoni yosankhidwa bwino inasangalatsidwa chifukwa cha zimenezi. (Sheol h7585)
(parallel missing)
Amene ankakhala mu mthunzi wake, amene ankayanjana nawo, iwonso anapita nawo pamodzi ku manda, kukakhala pamodzi ndi amene anaphedwa ndi lupanga pakati pa mitundu ya anthu. (Sheol h7585)
(parallel missing)
Mʼkati mwa manda atsogoleri amphamvu pamodzi ndi ogwirizana nawo azidzakambirana za Igupto nʼkumati, ‘Afika kuno anthu osachita mdulidwe aja! Ndi awa agona apawa, ophedwa pa nkhondo.’ (Sheol h7585)
(parallel missing)
Iwo sanayikidwe mwaulemu ngati ankhondo amphamvu amakedzana, amene anatsikira ku dziko la anthu akufa ndi zida zawo zomwe za nkhondo. Malupanga awo anawayika ku mitu yawo, ndipo zishango zawo anaphimba mafupa awo. Kale anthu amphamvu amenewa ankaopsa dziko la anthu amoyo. (Sheol h7585)
(parallel missing)
“Ndidzawapulumutsa ku mphamvu ya manda; ndidzawawombola ku imfa. Kodi iwe imfa, miliri yako ili kuti? Kodi iwe manda, kuwononga kwako kuli kuti? “Sindidzachitanso chifundo, (Sheol h7585)
(parallel missing)
Ngakhale atakumba pansi mpaka ku malo a anthu akufa, dzanja langa lidzawatulutsa kumeneko. Ngakhale atakwera kumwamba Ine ndidzawatsakamutsa kumeneko. (Sheol h7585)
(parallel missing)
Iye anati: “Pamene ndinali mʼmavuto anga ndinayitana Yehova, ndipo Iye anandiyankha. Ndili ku dziko la anthu akufa ndinapempha thandizo, ndipo Inu munamva kulira kwanga. (Sheol h7585)
(parallel missing)
Ndithu, wasokonezeka ndi vinyo; ndi wodzitama ndiponso wosakhazikika. Pakuti ngodzikonda ngati manda, ngosakhutitsidwa ngati imfa, wadzisonkhanitsira mitundu yonse ya anthu ndipo wagwira ukapolo anthu a mitundu yonse. (Sheol h7585)
(parallel missing)
Koma Ine ndikukuwuzani kuti aliyense wokwiyira mʼbale wake adzapezeka wolakwa ku bwalo la milandu. Ndiponso aliyense amene wonena mʼbale wake kuti, ‘Ndiwe wopanda phindu,’ adzapezeka wolakwa ku bwalo la milandu lalikulu. Ndipo aliyense amene anganene mnzake ‘wopandapake’ adzatengeredwa ku bwalo la milandu. Ndiponso aliyense amene angamunene mnzake kuti, ‘Chitsiru iwe,’ adzaponyedwa ku gehena. (Geenna g1067)
Dar Eu vă spun că oricine se mânie pe fratele său fără motiv va fi în primejdie de judecată. Oricine îi va spune fratelui său: “Raca!” va fi în pericol de consiliu. Oricine îi va spune: “Prostule!” va fi în pericol de focul gheenei. (Geenna g1067)
Ngati diso lako lakumanja likuchimwitsa, ulichotse ndi kulitaya. Pakuti nʼkwabwino kwa iwe kutaya chiwalo chimodzi cha thupi lako, kusiyana ndi kuti thupi lonse liponyedwe mʼgehena. (Geenna g1067)
Dacă ochiul tău drept te face să te poticnești, smulge-l și aruncă-l de la tine. Căci este mai de folos să piară unul dintre membrele tale decât ca tot trupul tău să fie aruncat în gheenă. (Geenna g1067)
Ndipo ngati dzanja lako lamanja likuchimwitsa, ulidule ndi kulitaya. Pakuti nʼkwabwino kwa iwe kutaya chiwalo chimodzi cha thupi lako, kusiyana ndi kuti thupi lonse liponyedwe mʼgehena. (Geenna g1067)
Dacă mâna ta dreaptă te face să te poticnești, taie-o și arunc-o departe de tine. Căci îți este mai de folos să piară unul din membrele tale, decât să fie aruncat tot trupul tău în Gheenă. (Geenna g1067)
Musamaope amene amapha thupi koma sangathe kuchotsa moyo. Koma muziopa Iye amene akhoza kupha mzimu ndi kuwononga thupi mu gehena. (Geenna g1067)
Nu vă temeți de cei care ucid trupul, dar nu pot ucide sufletul. Temeți-vă mai degrabă de cel care este în stare să nimicească și sufletul și trupul în Gheenă. (Geenna g1067)
Ndipo iwe Kaperenawo, kodi udzakwezedwa kufika kumwamba? Ayi, udzatsitsidwa mpaka pansi kufika ku Hade. Ngati zodabwitsa zimene zinachitika mwa iwe, zikanachitika mu Sodomu, bwenzi iye alipo kufikira lero. (Hadēs g86)
Tu, Capernaum, care te-ai înălțat la cer, te vei coborî în Hades. Căci, dacă s-ar fi făcut în Sodoma lucrările mărețe care s-au făcut în voi, ar fi rămas până astăzi. (Hadēs g86)
Aliyense amene anena mawu otsutsana ndi Mwana wa Munthu adzakhululukidwa koma aliyense wonena motsutsana ndi Mzimu Woyera sadzakhululukidwa mu mʼbado uno kapena umene ukubwerawo. (aiōn g165)
Oricine va spune un cuvânt împotriva Fiului Omului, îi va fi iertat, dar oricine va vorbi împotriva Duhului Sfânt, nu-i va fi iertat, nici în veacul acesta, nici în cel viitor. (aiōn g165)
Zimene zinafesedwa pakati pa minga, ndi munthu amene amamva mawu koma nkhawa za moyo uno ndi chinyengo cha chuma zimalepheretsa mawuwo kuti abale chipatso. (aiōn g165)
Ceea ce a fost semănat între spini, acesta este cel care ascultă cuvântul, dar grijile veacului acestuia și înșelăciunea bogățiilor înăbușă cuvântul, și el devine neînsuflețit. (aiōn g165)
Ndipo amene anafesa namsongole ndi Satana. Kukolola ndiko kutha kwa dzikoli ndipo otuta ndi angelo. (aiōn g165)
Dușmanul care le-a semănat este diavolul. Secerișul este sfârșitul veacului, iar secerătorii sunt îngerii. (aiōn g165)
“Monga momwe namsongole azulidwa ndi kutenthedwa ndi moto, momwemonso kudzakhala pakutha kwa dziko. (aiōn g165)
De aceea, așa cum buruienile de scorbură sunt adunate și arse în foc, așa va fi și la sfârșitul acestui veac. (aiōn g165)
Umu ndi mmene kudzakhalira pakutha kwa dziko. Angelo adzabwera ndi kulekanitsa oyipa ndi olungama. (aiōn g165)
Așa va fi și la sfârșitul lumii. Îngerii vor veni și îi vor despărți pe cei răi dintre cei drepți (aiōn g165)
Ndipo Ine ndikuwuza iwe kuti ndiwe Petro ndipo pa thanthwe ili Ine ndidzamangapo mpingo wanga ndipo makomo a ku gehena sadzawugonjetsa. (Hadēs g86)
Îți spun și Eu îți spun că tu ești Petru și pe această piatră voi zidi Adunarea Mea și porțile Hadesului nu o vor birui. (Hadēs g86)
Ngati dzanja lako kapena phazi lako likuchimwitsa, lidule ndi kulitaya. Ndi bwino kwa iwe kulowa mʼmoyo wosatha wolumala kusiyana ndi kukhala ndi manja awiri kapena mapazi awiri ndi kukaponyedwa ku moto wosatha. (aiōnios g166)
Dacă mâna sau piciorul tău te face să te poticnești, taie-le și leapădă-le de la tine. Este mai bine pentru tine să intri în viață mutilat sau schilodit, decât să ai două mâini sau două picioare pentru a fi aruncat în focul veșnic. (aiōnios g166)
Ndipo ngati diso lako likuchimwitsa, ulichotse ndi kulitaya. Ndi bwino kwa iwe kuti ukalowe ku moyo wosatha ndi diso limodzi kuposa ndi kukhala ndi maso awiri ndi kukaponyedwa ku moto wa gehena.” (Geenna g1067)
Dacă ochiul tău te face să te poticnești, smulge-l și aruncă-l de la tine. Este mai bine pentru tine să intri în viață cu un singur ochi, decât să ai doi ochi pentru a fi aruncat în gheena de foc. (Geenna g1067)
Taonani mnyamata wina anabwera kwa Yesu namufunsa kuti, “Aphunzitsi, ndi chinthu chiti chabwino chimene ndiyenera kuchita kuti ndipeze moyo wosatha?” (aiōnios g166)
Și iată că a venit cineva la El și a zis: “Învățătorule, ce să fac ca să am viața veșnică?” (aiōnios g166)
Ndipo aliyense amene wasiya nyumba, kapena abale, kapena alongo, kapena bambo kapena mayi kapena mkazi, kapena ana, kapena minda chifukwa cha Ine adzalandira madalitso ochuluka ndi kulandiranso moyo wosatha. (aiōnios g166)
Oricine a lăsat case, sau frați, sau surori, sau tată, sau mamă, sau soție, sau copii, sau pământuri, de dragul numelui Meu, va primi de o sută de ori și va moșteni viața veșnică. (aiōnios g166)
Ataona mtengo wamkuyu mʼmbali mwa msewu, anapitapo koma sanapeze kanthu koma masamba okhaokha. Pamenepo anati kwa mtengowo, “Usadzabalenso chipatso!” Nthawi yomweyo mtengowo unafota. (aiōn g165)
Văzând un smochin lângă drum, s-a apropiat de el și n-a găsit pe el decât frunze. I-a spus: “Să nu mai fie niciun fruct de la tine în veci!” Imediat smochinul s-a uscat. (aiōn g165)
“Tsoka kwa inu, aphunzitsi amalamulo ndi Afarisi, achiphamaso! Mumayenda maulendo ambiri pa mtunda ndi pa nyanja kuti mutembenuze munthu mmodzi, ndipo akatembenuka, mumamusandutsa kukhala mwana wa gehena kawiri kuposa inu. (Geenna g1067)
Vai vouă, cărturari și farisei, ipocriților! Pentru că voi călătoriți pe mare și pe uscat ca să faceți un singur proselit; și când acesta devine unul, îl faceți de două ori mai fiu al Gheenei decât voi înșivă. (Geenna g1067)
“Njoka inu! Ana amamba! Mudzachithawa bwanji chilango cha gehena? (Geenna g1067)
Voi, șerpi, urmași ai viperelor, cum veți scăpa de judecata Gheenei? (Geenna g1067)
Pamene Yesu anakhala pansi pa phiri la Olivi, ophunzira ake anabwera kwa Iye mwamseri nati, “Tiwuzeni, kodi izi zidzachitika liti, ndipo chizindikiro cha kubwera kwanu ndi zizindikiro za kutha kwa dziko zidzakhala chiyani?” (aiōn g165)
Pe când ședea El pe Muntele Măslinilor, ucenicii au venit la El în particular și I-au zis: “Spune-ne, când se vor întâmpla aceste lucruri? Care este semnul venirii Tale și al sfârșitului veacului?” (aiōn g165)
“Pamenepo adzanena kwa akumanzere kwake kuti, ‘Chokani kwa Ine, inu otembereredwa, pitani ku moto wosatha wokonzedwera mdierekezi ndi angelo ake. (aiōnios g166)
Apoi va spune și celor de la stânga: 'Duceți-vă de la Mine, blestemaților, în focul cel veșnic, pregătit diavolului și îngerilor lui; (aiōnios g166)
“Amenewa adzapita ku chilango chosatha pamene olungama ku moyo wosatha.” (aiōnios g166)
Aceștiavor pleca la pedeapsa veșnică, dar cei drepți la viața veșnică.” (aiōnios g166)
ndi kuwaphunzitsa amvere zonse zimene ndinakulamulirani. Ndipo onani, Ine ndidzakhala pamodzi ndi inu kufikira kutha kwa dziko lapansi pano.” (aiōn g165)
învățându-isă păzească toate lucrurile pe care vi le-am poruncit. Iată, Eu sunt cu voi în toate zilele, până la sfârșitul veacului.” Amin. (aiōn g165)
koma aliyense amene achitira mwano Mzimu Woyera sadzakhululukidwa pakuti wachita tchimo losatha.” (aiōn g165, aiōnios g166)
dar oricine va huli împotriva Duhului Sfânt nu va avea iertare, ci va fi supus osândei veșnice.” (aiōn g165, aiōnios g166)
koma nkhawa zamoyo uno, chinyengo cha chuma ndi zokhumba za zinthu zina zimabwera ndi kutchinga mawu, ndipo amawachititsa kukhala osabala chipatso. (aiōn g165)
dar grijile acestui veac, înșelăciunea bogățiilor și poftele altor lucruri care intră în el înăbușă cuvântul și acesta devine neînsuflețit. (aiōn g165)
Ngati dzanja lako likuchimwitsa, lidule. Ndi kwabwino kwa iwe kulowa mʼmoyo ndi dzanja limodzi kusiyana ndi kukhala ndi manja awiri ndi kupita ku gehena, kumene moto wake suzima. (Geenna g1067)
Dacă mâna ta te face să te poticnești, taie-ți-o! Este mai bine pentru tine să intri în viață mutilat, decât să ai cele două mâini pentru a merge în Gheena, în focul nestins, (Geenna g1067)
Ndipo ngati phazi lako likuchimwitsa, lidule. Ndi kwabwino kwa iwe kulowa mʼmoyo olumala kusiyana ndi kukhala ndi mapazi awiri ndi kuponyedwa mu gehena. (Geenna g1067)
Dacă piciorul tău te face să te poticnești, taie-l! Este mai bine pentru tine să intri în viață șchiop, decât ca cele două picioare să fie aruncate în Gheena, în focul care nu se va stinge niciodată — (Geenna g1067)
Ndipo ngati diso lako likuchimwitsa, likolowole. Ndi kwabwino kwa iwe kulowa ufumu wa Mulungu ndi diso limodzi, kusiyana ndi kukhala ndi maso awiri ndi kuponyedwa mu gehena, (Geenna g1067)
Dacă ochiul tău te face să te poticnești, aruncă-l afară. Este mai bine pentru tine să intri în Împărăția lui Dumnezeu cu un singur ochi, decât să ai doi ochi pentru a fi aruncat în Gheena de foc, (Geenna g1067)
Yesu atanyamuka, munthu wina anamuthamangira nagwa mogwada pamaso pake. Iye anafunsa kuti, “Aphunzitsi abwino, ndichite chiyani kuti ndilandire moyo wosatha?” (aiōnios g166)
Pe când ieșea El pe cale, a alergat unul la El, a îngenuncheat înaintea Lui și L-a întrebat: “Învățătorule, ce să fac ca să moștenesc viața veșnică?” (aiōnios g166)
adzalephera kulandira 100 (nyumba, abale, alongo, amayi, ana ndi minda, pamodzi ndi mazunzo) mʼbado uno ndi moyo wosatha nthawi ya mʼtsogolo. (aiōn g165, aiōnios g166)
ci va primi de o sută de ori mai mult acum, în veacul acesta: case, frați, surori, mame, copii, pământ, cu prigoane, iar în veacul viitor, viața veșnică. (aiōn g165, aiōnios g166)
Ndipo Iye anati kwa mtengo, “Palibe amene adzadyenso chipatso kuchokera kwa iwe.” Ndipo ophunzira ake anamva Iye akunena izi. (aiōn g165)
Isus i-a spus: “Fie ca nimeni să nu mai mănânce vreodată fructe de la tine!”, iar discipolii lui au auzit. (aiōn g165)
ndipo adzalamulira pa nyumba ya Yakobo ku nthawi zonse; ufumu wake sudzatha.” (aiōn g165)
și va domni peste casa lui Iacov pentru totdeauna. Împărăția lui nu va avea sfârșit”. (aiōn g165)
Kwa Abrahamu ndi zidzukulu zake ku nthawi zonse monga ananena kwa makolo athu.” (aiōn g165)
așa cum a vorbit părinților noștri, lui Avraam și urmașilor lui în veci.” (aiōn g165)
(Monga mmene ananenera kudzera mwa aneneri oyera), (aiōn g165)
(așa cum a vorbit prin gura sfinților Săi prooroci care au fost din vechime), (aiōn g165)
Ndipo ziwandazo zimamupempha mobwerezabwereza kuti asazitumize ku dzenje la mdima. (Abyssos g12)
Ei l-au implorat să nu le poruncească să se ducă în abis. (Abyssos g12)
Kodi iwe Kaperenawo, adzakukweza mpaka kumwamba? Ayi, adzakutsitsa mpaka ku Malo a anthu akufa. (Hadēs g86)
Tu, Capernaum, care te-ai înălțat la cer, vei fi coborât în Hades. (Hadēs g86)
Nthawi ina katswiri wa malamulo anayimirira kuti ayese Yesu. Iye anati, “Aphunzitsi, ndichite chiyani kuti ndikhale ndi moyo wosatha?” (aiōnios g166)
Și iată că un învățător s-a ridicat în picioare și L-a pus la încercare, zicând: “Învățătorule, ce să fac ca să moștenesc viața veșnică?” (aiōnios g166)
Koma Ine ndidzakuonetsani amene muyenera kumuopa: Wopani Iye, amene pambuyo pakupha thupi, ali ndi mphamvu yakukuponyani ku gehena. Inde, Ine ndikuwuzani, muopeni Iye. (Geenna g1067)
Ci vă voi avertiza de cine trebuie să vă temeți. Temeți-vă de cel care, după ce a ucis, are puterea de a arunca în Gheenă. Da, vă spun, temeți-vă de el. (Geenna g1067)
“Bwana anayamikira kapitawo wosakhulupirikayo popeza anachita mochenjera. Pakuti anthu a dziko lino lapansi ndi ochenjera kwambiri akamachita zinthu ndi anthu ofanana nawo kuposa anthu a kuwunika. (aiōn g165)
“Domnul său l-a lăudat pe administratorul necinstit pentru că a procedat cu înțelepciune, căci copiii acestei lumi sunt, în neamul lor, mai înțelepți decât copiii luminii. (aiōn g165)
Ine ndikukuwuzani inu, gwiritsani ntchito chuma cha dziko lapansi kuti mudzipezere nokha abwenzi, kuti pamene chatha mudzalandiridwe mʼmalo okhala amuyaya. (aiōnios g166)
Eu vă spun: faceți-vă prieteni prin intermediul bogățiilor nedrepte, pentru ca, atunci când veți eșua, ei să vă primească în corturile veșnice. (aiōnios g166)
Ali mʼgehena kuzunzika, anakweza maso ake ndipo anaona Abrahamu ali ndi Lazaro pambali pake. (Hadēs g86)
În Hades, și-a ridicat ochii, fiind în chinuri, și a văzut departe pe Avraam și pe Lazăr la sânul lui. (Hadēs g86)
Oweruza wina wake anamufunsa Iye kuti, “Aphunzitsi abwino, ndichite chiyani kuti ndilandire moyo wosatha?” (aiōnios g166)
Un domnitor L-a întrebat: “Învățătorule, ce să fac ca să moștenesc viața veșnică?” (aiōnios g166)
adzalephera kulandira mowirikiza mʼmoyo uno, ndi mʼmoyo ukubwerawo, moyo wosatha.” (aiōn g165, aiōnios g166)
care să nu primească de multe ori mai mult în acest timp și în lumea viitoare viața veșnică.” (aiōn g165, aiōnios g166)
Yesu anayankha kuti, “Anthu a mʼbado uno amakwatira ndi kukwatiwa. (aiōn g165)
Isus le-a zis: “Copiii veacului acestuia se căsătoresc și sunt dați în căsătorie. (aiōn g165)
Koma mʼmoyo umene ukubwerawo, anthu amene adzaukitsidwe kwa akufa sadzakwatira kapena kukwatiwa. (aiōn g165)
Dar cei care sunt considerați vrednici să ajungă la vârsta aceea și la învierea din morți nu se căsătoresc și nici nu sunt dați în căsătorie. (aiōn g165)
kuti aliyense amene akhulupirira Iye akhale ndi moyo wosatha. (aiōnios g166)
pentru ca oricine crede în el să nu piară, ci să aibă viață veșnică. (aiōnios g166)
“Pakuti Mulungu anakonda dziko lapansi, kotero anapereka Mwana wake wobadwa yekha, kuti aliyense wokhulupirira Iye asatayike koma akhale ndi moyo wosatha. (aiōnios g166)
Fiindcă atât de mult a iubit Dumnezeu lumea, încât a dat pe singurul Său Fiu născut, pentru ca oricine crede în El să nu piară, ci să aibă viață veșnică. (aiōnios g166)
Aliyense wokhulupirira Mwanayo ali ndi moyo wosatha, koma iye amene samvera Mwanayo sadzawuona moyo, pakuti mkwiyo wa Mulungu umakhala pa iye.” (aiōnios g166)
Cine crede în Fiul are viață veșnică, dar cine nu ascultă de Fiul nu va vedea viața, ci mânia lui Dumnezeu rămâne asupra lui.” (aiōnios g166)
koma aliyense amene adzamwa madzi amene Ine ndidzamupatsa sadzamvanso ludzu. Ndithudi, madzi amene ndidzamupatsa adzakhala kasupe wamadzi wotumphukira ku moyo wosatha.” (aiōn g165, aiōnios g166)
dar oricine va bea din apa pe care i-o voi da Eu, nu va mai înseta niciodată, ci apa pe care i-o voi da Eu va deveni în el un izvor de apă care izvorăște pentru viața veșnică.” (aiōn g165, aiōnios g166)
Ngakhale tsopano amene akukolola akulandira malipiro ake, ndipo akututa mbewu ku moyo wosatha kuti wofesa ndi wokolola asangalale pamodzi. (aiōnios g166)
Cel care seceră primește plata și culege roade pentru viața veșnică, pentru ca atât cel care seamănă, cât și cel care seceră să se bucure împreună. (aiōnios g166)
“Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti aliyense amene amamva mawu anga ndi kukhulupirira Iye amene ananditumiza Ine, ali ndi moyo wosatha ndipo sadzaweruzidwa. Iye wachoka mu imfa ndipo walowa mʼmoyo. (aiōnios g166)
“Adevărat vă spun că cine ascultă cuvântul Meu și crede pe Cel ce M-a trimis pe Mine are viață veșnică și nu vine la judecată, ci a trecut din moarte la viață. (aiōnios g166)
Inu mumasanthula malemba chifukwa mumaganiza kuti mʼmalembamo muli moyo wosatha. Awa ndi malemba amene akundichitira umboni. (aiōnios g166)
Voi cercetați Scripturile, pentru că credeți că în ele aveți viața veșnică; și acestea sunt cele ce mărturisesc despre Mine. (aiōnios g166)
Gwirani ntchito, osati chifukwa cha chakudya chimene chimawonongeka koma chifukwa cha chakudya chimene sichiwonongeka mpaka ku moyo wosatha, chimene Mwana wa Munthu adzakupatsani. Mulungu Atate anamusindikiza chizindikiro chomuvomereza.” (aiōnios g166)
Nu lucrați pentru hrana care piere, ci pentru hrana care rămâne pentru viața veșnică, pe care v-o va da Fiul Omului. Căci Dumnezeu Tatăl l-a pecetluit.” (aiōnios g166)
Pakuti chifuniro cha Atate anga ndi chakuti aliyense amene aona Mwanayo namukhulupirira akhale ndi moyo wosatha, ndipo Ine ndidzamuukitsa kwa akufa pa tsiku lomaliza.” (aiōnios g166)
Aceasta este voia Celui care m-a trimis: ca oricine vede pe Fiul și crede în El să aibă viața veșnică; și Eu îl voi învia în ziua de apoi.” (aiōnios g166)
Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti Iye amene akhulupirira ali nawo moyo wosatha. (aiōnios g166)
Adevărat, vă spun, cel ce crede în Mine are viața veșnică. (aiōnios g166)
Ine ndine chakudya chamoyo chochokera kumwamba. Ngati munthu adya chakudya ichi, adzakhala ndi moyo nthawi zonse. Chakudya chimenechi ndi thupi langa, limene Ine ndidzalipereka kuti anthu pa dziko lapansi akhale ndi moyo.” (aiōn g165)
Eu sunt pâinea vie care s-a coborât din cer. Dacă cineva mănâncă din pâinea aceasta, va trăi în veci. Da, pâinea pe care o voi da pentru viața lumii este carnea mea.” (aiōn g165)
Aliyense amene adya thupi langa ndi kumwa magazi anga ali ndi moyo wosatha ndipo Ine ndidzamuukitsa kwa akufa pa tsiku lomaliza. (aiōnios g166)
Cine mănâncă carnea Mea și bea sângele Meu are viață veșnică și Eu îl voi învia în ziua de apoi. (aiōnios g166)
Ichi ndiye chakudya chimene chinatsika kuchokera kumwamba. Makolo athu akale anadya mana ndi kufa, koma iye amene adya chakudya ichi, adzakhala ndi moyo nthawi yonse.” (aiōn g165)
Aceasta este pâinea care s-a coborât din cer — nu cum au mâncat părinții noștri mana și au murit. Cel care mănâncă această pâine va trăi în veci.” (aiōn g165)
Simoni Petro anamuyankha Iye kuti, “Ambuye, ife tidzapita kwa yani? Inu muli ndi mawu amoyo wosatha. (aiōnios g166)
Simon Petru I-a răspuns: “Doamne, la cine să mergem? Tu ai cuvintele vieții veșnice. (aiōnios g166)
Pajatu kapolo alibe malo wokhazikika mʼbanja, koma mwana ndi wa mʼbanjamo nthawi zonse. (aiōn g165)
O roabă nu locuiește în casă pentru totdeauna. Un fiu rămâne pentru totdeauna. (aiōn g165)
Ine ndikukuwuzani choonadi, munthu akasunga mawu anga, sadzafa konse.” (aiōn g165)
Mai mult ca sigur, vă spun că, dacă o persoană respectă cuvântul meu, nu va vedea niciodată moartea.” (aiōn g165)
Pamenepo Ayuda anafuwula kuti, “Tsopano ife tadziwadi kuti Inu ndi wogwidwa ndi chiwanda! Abrahamu anafa ndiponso aneneri, koma Inu mukunena kuti, ‘Ngati munthu asunga mawu anga, sadzafa.’ (aiōn g165)
Atunci iudeii i-au zis: “Acum știm că ai un demon. Avraam a murit, ca și profeții, iar tu spui: “Dacă un om păzește cuvântul Meu, nu va gusta niciodată moartea”. (aiōn g165)
Palibe amene anamvapo za kutsekula maso a munthu wobadwa wosaona. (aiōn g165)
De la începutul lumii nu s-a auzit niciodată ca cineva să fi deschis ochii unui orb din naștere. (aiōn g165)
Ine ndimazipatsa moyo wosatha ndipo sizidzawonongeka. Palibe amene adzazikwatula mʼdzanja langa. (aiōn g165, aiōnios g166)
Eu le dau viața veșnică. Ele nu vor pieri niciodată și nimeni nu le va smulge din mâna mea. (aiōn g165, aiōnios g166)
Aliyense amene ali ndi moyo ndi kukhulupirira Ine sadzamwalira. Kodi iwe ukukhulupirira izi?” (aiōn g165)
Oricine trăiește și crede în Mine nu va muri niciodată. Crezi tu asta?” (aiōn g165)
Munthu amene amakonda moyo wake adzawutaya, pamene munthu amene amadana ndi moyo wake mʼdziko lino lapansi adzawusungira ku moyo wosatha. (aiōnios g166)
Cine își iubește viața o va pierde. Cel care își urăște viața în lumea aceasta o va păstra pentru viața veșnică. (aiōnios g166)
Gulu la anthu linayankha kuti, “Ife tinamva kuchokera mʼmalamulo kuti Khristu adzakhala kwamuyaya, nanga bwanji Inu mukunena kuti, ‘Mwana wa Munthu ayenera kukwezedwa?’ Kodi Mwana wa Munthuyu ndani?” (aiōn g165)
Și mulțimea i-a răspuns: “Am auzit din Lege că Hristosul rămâne pentru totdeauna. Cum spuneți voi: 'Fiul Omului trebuie să fie înălțat'? Cine este acest Fiu al Omului?” (aiōn g165)
Ine ndikudziwa kuti lamulo lake ndi moyo wosatha. Choncho chilichonse chimene Ine ndinena ndi chimene Atate andiwuza.” (aiōnios g166)
Știu că porunca Lui este viața veșnică. Așadar, lucrurile pe care le spun, așa cum mi-a spus Tatăl, așa vorbesc și eu.” (aiōnios g166)
Petro anati, “Ayi, Inu simudzandisambitsa konse mapazi anga.” Yesu anayankha kuti, “Ngati Ine sindisambitsa mapazi ako, ulibe gawo mwa Ine.” (aiōn g165)
Petru i-a zis: “Nu-mi vei spăla niciodată picioarele!” Isus i-a răspuns: “Dacă nu te spăl, nu ai parte cu Mine”. (aiōn g165)
Ine ndidzapempha Atate, ndipo adzakupatsani Nkhoswe ina kuti izikhala nanu nthawi zonse. (aiōn g165)
Eu mă voi ruga Tatălui și el vă va da un alt Sfetnic, ca să fie cu voi în veci: (aiōn g165)
Pakuti Inu munamupatsa Iye ulamuliro pa anthu onse kuti apereke moyo wosatha kwa onse amene mwamupatsa. (aiōnios g166)
așa cum i-ai dat autoritate peste toată făptura, așa va da viață veșnică tuturor celor pe care i-ai dat-o. (aiōnios g166)
Tsono moyo wosathawo ndi uwu: Iwo akudziweni Inu, Mulungu yekhayo woona, ndi Yesu Khristu, amene Inu mwamutuma. (aiōnios g166)
Aceasta este viața veșnică: să te cunoască pe tine, singurul Dumnezeu adevărat, și pe cel pe care l-ai trimis, Isus Hristos. (aiōnios g166)
Chifukwa simudzasiya moyo wanga kumalo a anthu akufa, ku manda, kapena kulekerera Woyerayo kuti awole. (Hadēs g86)
pentru că nu vei lăsa sufletul meu în Locuința morților, nici nu vei permite ca Sfântul tău să vadă putreziciunea. (Hadēs g86)
Davide ataoneratu zimene zinali mʼtsogolo anayankhula za kuuka kwa Khristu, kuti Iye sanasiyidwe mʼmanda, ndipo thupi lake silinawole. (Hadēs g86)
el, prevăzând acest lucru, a vorbit despre învierea lui Hristos, că sufletul lui nu a rămas în Hades și că trupul lui nu a văzut putrezirea. (Hadēs g86)
Iye ayenera kukhalabe kumwamba mpaka nthawi ya kukonzanso zinthu zonse monga Mulungu analonjeza kale kudzera mwa aneneri ake oyera mtima. (aiōn g165)
pe care cerul trebuie să-L primească până la vremurile de refacere a tuturor lucrurilor, pe care Dumnezeu le-a spus demult prin gura sfinților Săi prooroci. (aiōn g165)
Ndipo Paulo ndi Barnaba anawayankha molimba mtima kuti, “Ife tinayenera kuyankhula Mawu a Mulungu kwa inu poyamba. Popeza inu mwawakana ndi kudziyesa nokha osayenera moyo wosatha, ife tsopano tikupita kwa anthu a mitundu ina. (aiōnios g166)
Pavel și Barnaba au luat cuvântul cu îndrăzneală și au zis: “Trebuia să vă fie vestit mai întâi cuvântul lui Dumnezeu. Întrucât, într-adevăr, îl respingeți de la voi înșivă și vă judecați nevrednici de viața veșnică, iată că ne întoarcem la neamuri. (aiōnios g166)
Anthu a mitundu ina atamva izi, anakondwa ndipo analemekeza Mawu Ambuye; ndipo onse amene anawasankha kuti alandire moyo osatha anakhulupirira. (aiōnios g166)
Neamurile, auzind acestea, s-au bucurat și au slăvit cuvântul lui Dumnezeu. Toți cei care erau rânduiți pentru viața veșnică au crezut. (aiōnios g166)
zinaululidwa kuyambira kalekale.’ (aiōn g165)
“Toate lucrările lui Dumnezeu sunt cunoscute de El din veșnicie. (aiōn g165)
Pakuti kuyambira pamene dziko lapansi linalengedwa, zinthu zosaoneka za Mulungu, mphamvu zake zosatha ndi chikhalidwe cha umulungu, zakhala zikuoneka bwinobwino. Akhala akuzindikira poona zimene Mulungu analenga, kotero kuti anthu sangathe kuwiringula. (aïdios g126)
Căci lucrurile invizibile ale Lui, de la crearea lumii, se văd în mod clar, fiind percepute prin lucrurile care sunt făcute, adică puterea Lui veșnică și divinitatea Lui, pentru ca ei să fie fără scuză. (aïdios g126)
Iwo anasinthanitsa choonadi cha Mulungu ndi bodza ndipo anapembedza ndi kutumikira zinthu zolengedwa mʼmalo mwa Mlengi amene ali woyenera kutamandidwa mpaka muyaya. Ameni. (aiōn g165)
care au schimbat adevărul lui Dumnezeu cu minciuna și s-au închinat și au slujit mai degrabă creaturii decât Creatorului, care este binecuvântat în veci. Amin. (aiōn g165)
Iye adzapereka moyo wosatha kwa amene amafunafuna ulemerero, ulemu ndi moyo pochita ntchito zabwino mopirira. (aiōnios g166)
celor care, prin perseverența în binele făcut, caută gloria, onoarea și incoruptibilitatea, viața veșnică; (aiōnios g166)
Choncho monga momwe tchimo linkalamulira anthu ndi kubweretsa imfa pa iwo, chomwecho kunali koyenera kuti chisomo chilamulire pobweretsa chilungamo kwa anthu, ndi kuwafikitsa ku moyo wosatha mwa Yesu Khristu Ambuye athu. (aiōnios g166)
pentru ca, după cum păcatul a domnit în moarte, tot așa harul să domnească prin dreptate pentru viața veșnică, prin Isus Hristos, Domnul nostru. (aiōnios g166)
Koma tsopano pakuti inu mwamasulidwa ku tchimo ndipo mwasanduka akapolo a Mulungu, phindu lomwe mulipeza ndi kuyera mtima ndipo chotsatira chake ndi moyo wosatha. (aiōnios g166)
Dar acum, fiind eliberați de păcat și deveniți robi ai lui Dumnezeu, aveți rodul sfințirii și rezultatul vieții veșnice. (aiōnios g166)
Pakuti malipiro a tchimo ndi imfa, koma mphatso yaulere imene Mulungu amapereka ndi moyo wosatha mwa Khristu Yesu Ambuye athu. (aiōnios g166)
Căci plata păcatului este moartea, dar darul gratuit al lui Dumnezeu este viața veșnică în Hristos Isus, Domnul nostru. (aiōnios g166)
Awo ndi makolo athu. Kuchokera kwa iwo mʼthupi ndi kumene kunachokera makolo a Khristu Yesu amene ndi Mulungu wolamulira zinthu zonse, alemekezeke mpaka muyaya! Ameni. (aiōn g165)
din care sunt părinții și din care provine Cristos în ceea ce privește trupul, care este peste toate, Dumnezeu, binecuvântat în veci. Amin. (aiōn g165)
“kapena ‘Ndani adzatsikira ku dziko la anthu akufa?’” (ndiko, kukamutenga Khristu kwa akufa). (Abyssos g12)
sau: “Cine se va coborî în abis?” (adică să-l coboare pe Cristos); sau: “Cine se va coborî în abis?”. (adică să-l aducă pe Hristos din morți).” (Abyssos g12)
Pakuti Mulungu anasandutsa anthu onse a mʼndende ya kusamvera kuti Iye akaonetse chifundo kwa onse. (eleēsē g1653)
Căci Dumnezeu i-a legat pe toți de neascultare, ca să aibă milă de toți. (eleēsē g1653)
Pakuti zinthu zonse nʼzochokera kwa Iye, nʼzolengedwa ndi Iye ndipo zimabweretsa ulemerero kwa Iye. Kwa Iye kukhale ulemerero mpaka muyaya! Ameni. (aiōn g165)
Căci din El, prin El și pentru El sunt toate lucrurile. A lui să fie gloria în veci! Amin. (aiōn g165)
Musafanizidwenso ndi makhalidwe a dziko lino koma musandulike pokonzanso maganizo anu. Ndipo mudzadziwa ndi kuzindikira chifuniro chabwino cha Mulungu chomwe ndi chokondweretsa ndi changwiro. (aiōn g165)
Nu vă potriviți cu lumea aceasta, ci transformați-vă prin înnoirea minții voastre, ca să puteți dovedi care este voia lui Dumnezeu, bună, plăcută și desăvârșită. (aiōn g165)
Tsopano kwa Iye amene ali ndi mphamvu yokhazikitsa monga mwa uthenga wanga wabwino ndikulalikidwa kwa Yesu Khristu, monga mwa vumbulutso lachinsinsi chobisika kwa nthawi yayitali, (aiōnios g166)
Și acum, Celui ce poate să vă întărească, după Buna Vestire a mea și după propovăduirea lui Isus Hristos, după descoperirea tainei, care a fost ținută ascunsă în veacuri îndelungate, (aiōnios g166)
koma tsopano chavumbulutsidwa ndi kudziwika kudzera mʼMalemba a uneneri mwa lamulo la Mulungu wosatha, kuti mitundu yonse ikhulupirire ndi kumvera Iye, (aiōnios g166)
dar care acum s-a descoperit și, prin Scripturile profeților, după porunca Dumnezeului veșnic, a fost făcută cunoscută tuturor neamurilor, pentru ascultarea credinței, (aiōnios g166)
kwa Mulungu yekhayo wanzeru kukhale ulemerero kwamuyaya kudzera mwa Yesu Khristu! Ameni. (aiōn g165)
pentru singurul și înțeleptul Dumnezeu, prin Isus Hristos, căruia I se cuvine slava în veci! Amin. (aiōn g165)
Munthu wanzeru ali kuti? Munthu wozama ndi maphunziro ali kuti? Munthu wodziwa zakuya zamakono ali kuti? Kodi Mulungu sanazipusitse nzeru za dziko lapansi? (aiōn g165)
Unde este înțeleptul? Unde este scribul? Unde este cel care discută în acest veac? Oare nu a făcut Dumnezeu nebună înțelepciunea acestei lumi? (aiōn g165)
Komabe ife timayankhula uthenga wa nzeru kwa okhwima, koma osati ndi nzeru ya mʼbado uno kapena ya olamula a mʼbado uno, amene mphamvu yawo ikutha. (aiōn g165)
Noi însă vorbim cu înțelepciune printre cei maturi, dar nu cu înțelepciunea lumii acesteia și nici cu cea a conducătorilor lumii acesteia, care sunt pe cale de dispariție. (aiōn g165)
Ayi, ife timayankhula za nzeru yobisika ya Mulungu, nzeru imene inabisidwa ndipo imene Mulungu anatikonzera mu ulemerero wathu isanayambe nthawi. (aiōn g165)
Ci noi vorbim înțelepciunea lui Dumnezeu în taină, înțelepciunea care a fost ascunsă, pe care Dumnezeu a rânduit-o mai dinainte de lumi, pentru gloria noastră, (aiōn g165)
Palibe olamulira aliyense wa mʼbado uno amene anamumvetsetsa popeza anakamumvetsetsa sakanamupachika Ambuye wa ulemerero. (aiōn g165)
și pe care nu a cunoscut-o niciunul dintre conducătorii acestei lumi. Căci, dacă ar fi știut-o, nu L-ar fi răstignit pe Domnul slavei. (aiōn g165)
Choncho musadzinyenge. Ngati wina wa inu akuganiza kuti ndi wanzeru pa mulingo wa mʼbado uno, ayenera kukhala “wopusa” kuti athe kukhala wanzeru. (aiōn g165)
Nimeni să nu se înșele pe sine însuși. Dacă cineva crede că este înțelept între voi în lumea aceasta, să se facă nebun, ca să devină înțelept. (aiōn g165)
Nʼchifukwa chake ngati zimene ine ndimadya zichititsa mʼbale wanga kugwa mu tchimo, sindidzadyanso chakudyacho kuti mʼbaleyo ndisamuchimwitse. (aiōn g165)
De aceea, dacă mâncarea îl face pe fratele meu să se poticnească, nu voi mai mânca carne în veci, ca să nu-l fac pe fratele meu să se poticnească. (aiōn g165)
Zinthu izi zinawachitikira kuti zikhale chitsanzo ndipo zinalembedwa kuti zikhale chenjezo kwa ife, amene tiyandikira nthawi ya kutha kwa zonse. (aiōn g165)
Toate aceste lucruri li s-au întâmplat lor ca exemplu și au fost scrise pentru învățătura noastră, asupra cărora au venit sfârșiturile veacurilor. (aiōn g165)
“Iwe imfa, kupambana kwako kuli kuti? Iwe imfa, ululu wako uli kuti?” (Hadēs g86)
“Moarte, unde este înțepătura ta? Hades, unde este victoria ta?” (Hadēs g86)
Mulungu wa dziko lapansi anachititsa khungu anthu osakhulupirira, kuti asathe kuona kuwala kwa Uthenga Wabwino umene umaonetsa ulemerero wa Khristu, amene ndi chifaniziro cha Mulungu. (aiōn g165)
în care dumnezeul acestei lumi a orbit mințile celor necredincioși, pentru ca lumina Bunei Vestiri a slavei lui Cristos, care este chipul lui Dumnezeu, să nu răsară asupra lor. (aiōn g165)
Pakuti masautso athu ndi opepuka ndi a kanthawi, koma akutitengera ulemerero wamuyaya umene ndi wopambana kwambiri. (aiōnios g166)
Căci necazul nostru ușor, care este de moment, ne lucrează din ce în ce mai mult o greutate veșnică de glorie, (aiōnios g166)
Motero sitiyangʼana zinthu zimene ndi zooneka ndi maso, koma zinthu zimene ndi zosaoneka. Pakuti zimene zimaoneka ndi zosakhalitsa, koma zimene sizioneka ndi zamuyaya. (aiōnios g166)
în timp ce noi nu ne uităm la lucrurile care se văd, ci la cele care nu se văd. Căci lucrurile care se văd sunt vremelnice, dar lucrurile care nu se văd sunt veșnice. (aiōnios g166)
Popeza tikudziwa kuti ngati msasa wa dziko lapansi umene tikukhalamo uwonongeka, tili ndi nyumba yochokera kwa Mulungu, nyumba yamuyaya yakumwamba, osati yomangidwa ndi manja a anthu. (aiōnios g166)
Căci știm că, dacă se va desființa cortul nostru pământesc, avem o clădire de la Dumnezeu, o casă nefăcută de mână, veșnică, în ceruri. (aiōnios g166)
Paja analemba kuti, “Wopereka mphatso zake mowolowamanja kwa osauka, chilungamo chake chimanka mpaka muyaya.” (aiōn g165)
După cum este scris, “S-a împrăștiat în străinătate. El a dat săracilor. Neprihănirea Lui rămâne pentru totdeauna.” (aiōn g165)
Mulungu, Atate a Ambuye Yesu, amene tiyenera kumutamanda nthawi zonse, akudziwa kuti sindikunama. (aiōn g165)
Dumnezeul și Tatăl Domnului Isus Hristos, cel binecuvântat în veci de veci, știe că nu mint. (aiōn g165)
Yesuyo anadzipereka yekha chifukwa cha machimo athu kuti atipulumutse ku njira za moyo woyipa uno, molingana ndi chifuniro cha Mulungu ndi Atate athu. (aiōn g165)
care S-a dat pe Sine însuși pentru păcatele noastre, ca să ne izbăvească din veacul acesta rău, după voia Dumnezeului și Tatălui nostru, (aiōn g165)
Ulemerero ukhale kwa Mulunguyo mpaka muyaya. Ameni. (aiōn g165)
căruia I se cuvine slava în vecii vecilor. Amin. (aiōn g165)
Pakuti amene amafesa zokondweretsa thupi lake la uchimo, kuchokera ku khalidwe limenelo adzakolola chiwonongeko; amene amafesa zokondweretsa Mzimu, kuchokera kwa Mzimu adzakolola moyo wosatha. (aiōnios g166)
Căci cine seamănă pentru carnea sa, din carne va secera corupție. Dar cel care seamănă pentru Duhul va secera din Duhul viața veșnică. (aiōnios g166)
Anamukhazika pamwamba pa ulamuliro onse ndi mafumu, mphamvu ndi ufumu, ndiponso pamwamba pa dzina lililonse limene angalitchule, osati nthawi ino yokha komanso imene ikubwerayo. (aiōn g165)
cu mult mai presus de orice stăpânire, autoritate, putere, domnie și orice nume care se numește, nu numai în acest veac, ci și în cel ce va să vină. (aiōn g165)
mmene inu munkakhalamo pamene munkatsatira njira za dziko lapansi ndi za ulamuliro waufumu wa mlengalenga, mzimu umene ukugwira ntchito tsopano mwa amene samvera. (aiōn g165)
în care umblați odinioară, după cursul acestei lumi, după prințul puterii aerului, duhul care lucrează acum în copiii neascultătorilor. (aiōn g165)
ndi cholinga chakuti mʼnthawi imene ikubwera, Iyeyo adzaonetse chuma choposa cha chisomo chake, choonetsedwa mwa kukoma mtima kwake kwa ife mwa Khristu Yesu. (aiōn g165)
pentru ca în veacurile viitoare să arate bogăția nespus de mare a harului Său în bunătatea Sa față de noi în Hristos Isus; (aiōn g165)
Ndinasankhidwa kuti ndifotokoze momveka bwino kwa munthu aliyense za chinsinsi chimenechi, chinsinsi chimene kuyambira kale chinali chobisika mwa Mulungu amene analenga zinthu zonse. (aiōn g165)
și să fac pe toți oamenii să vadă care este administrarea misterului care de veacuri a fost ascuns în Dumnezeu, care a creat toate lucrurile prin Isus Hristos, (aiōn g165)
Chimenechi chinali chikonzero chamuyaya cha Mulungu, chimene chinachitika kudzera mwa Khristu Yesu Ambuye athu. (aiōn g165)
conform scopului veșnic pe care l-a împlinit în Hristos Isus, Domnul nostru. (aiōn g165)
Iyeyo akhale ndi ulemu mu mpingo ndi mwa Khristu Yesu pa mibado yonse mpaka muyaya. Ameni. (aiōn g165)
Lui să fie slava în adunare și în Hristos Isus, în toate generațiile, în vecii vecilor. Amin. (aiōn g165)
Pakuti sitikulimbana ndi thupi ndi magazi, koma tikulimbana ndi maufumu, maulamuliro, mphamvu za dziko la mdima, ndi mphamvu zoyipa kwambiri zauzimu zamlengalenga. (aiōn g165)
Căci lupta noastră nu este împotriva cărnii și a sângelui, ci împotriva principatelor, împotriva puterilor, împotriva stăpânitorilor lumii, a întunericului acestui veac și împotriva forțelor spirituale ale răutății din locurile cerești. (aiōn g165)
Kwa Mulungu ndi Atate athu, kukhale ulemerero mpaka muyaya. Ameni. (aiōn g165)
Acum, a Dumnezeului și Tatălui nostru să fie gloria în vecii vecilor! Amin. (aiōn g165)
chinsinsi chimene chakhala chikubisika kwa nthawi ndi mibado, koma tsopano chawululidwa kwa oyera mtima. (aiōn g165)
taina care a fost ascunsă de veacuri și de generații. Dar acum a fost descoperit sfinților Săi, (aiōn g165)
Adzalangidwa ndi chiwonongeko chamuyaya ndipo sadzaonanso nkhope ya Ambuye ndi ulemerero wamphamvu zake (aiōnios g166)
care va plăti pedeapsa: distrugerea veșnică de la fața Domnului și de la gloria puterii sale, (aiōnios g166)
Ambuye athu Yesu Khristu mwini ndi Mulungu Atate wathu, amene anatikonda ife ndipo mwachisomo chake anatipatsa kulimba mtima kwamuyaya ndi chiyembekezo chabwino, (aiōnios g166)
Iar Domnul nostru Iisus Hristos însuși și Dumnezeu Tatăl nostru, care ne-a iubit și ne-a dat prin har mângâierea veșnică și buna nădejde, (aiōnios g166)
Ndipo pa chifukwa chimenechi, Mulungu anandichitira chifundo, kuti mwa ine, wochimwitsitsa, Khristu Yesu aonetse kuleza mtima kwake konse kuti ndikhale chitsanzo cha omwe angathe kumukhulupirira ndi kulandira moyo wosatha. (aiōnios g166)
Totuși, din această cauză am obținut îndurare, pentru ca, în mine mai întâi, Isus Hristos să-și arate toată răbdarea ca exemplu pentru cei care urmau să creadă în el pentru viața veșnică. (aiōnios g166)
Tsopano kwa Mfumu yamuyaya, yosafa, yosaoneka, amene Iye yekha ndiye Mulungu, kukhale ulemu ndi ulemerero mpaka muyaya. Ameni. (aiōn g165)
Acum, Regelui veșnic, nemuritor și invizibil, lui Dumnezeu, care este singurul înțelept, să fie cinstea și gloria în vecii vecilor. Amin. (aiōn g165)
Menya nkhondo yabwino yachikhulupiriro. Gwiritsitsa moyo wosatha umene anakuyitanira pamene unavomereza bwino lomwe pamaso pa mboni zambiri. (aiōnios g166)
Luptă lupta cea bună a credinței. Apucă-te de viața veșnică la care ai fost chemat și ai mărturisit buna mărturisire în fața multor martori. (aiōnios g166)
Ndiye yekha wosafa ndipo amakhala mʼkuwala koopsa. Mulungu amene munthu aliyense sanamuone. Kwa Iye kukhale ulemu ndi mphamvu mpaka muyaya. Ameni. (aiōnios g166)
El singur are nemurirea, care locuiește într-o lumină de neatins, pe care nimeni nu l-a văzut și nici nu poate să-l vadă, căruia i se cuvine cinstea și puterea veșnică. Amin. (aiōnios g166)
Anthu onse amene ali ndi chuma uwalamule kuti asanyade kapena kuyika mitima yawo pa chuma chimene nʼchosadalirika. Koma chiyembekezo chawo chikhale mwa Mulungu amene amatipatsa mowolowamanja zonse zotisangalatsa. (aiōn g165)
Îndemnați-i pe cei ce sunt bogați în veacul acesta să nu se îngâmfe și să nu-și pună nădejdea în bogăția nesigură, ci în Dumnezeul cel viu, care ne dăruiește din belșug toate cele de care ne putem bucura; (aiōn g165)
Iye anatipulumutsa ndipo anatiyitanira ku moyo oyera mtima, osati chifukwa cha chilichonse chimene tinachita, koma chifukwa cha chikonzero ndi chisomo chake. Chisomo chimenechi anatipatsa ife mwa Khristu Yesu nthawi isanayambe. (aiōnios g166)
care ne-a salvat și ne-a chemat cu o chemare sfântă, nu după faptele noastre, ci după propriul său scop și har, care ne-a fost dat în Isus Hristos înainte de veșnicie, (aiōnios g166)
Choncho ndikupirira chilichonse chifukwa cha osankhidwa, kuti nawonso apulumutsidwe ndi Khristu Yesu ndi kulandira ulemerero wosatha. (aiōnios g166)
De aceea îndur toate lucrurile de dragul celor aleși, pentru ca și ei să dobândească mântuirea care este în Cristos Isus cu glorie veșnică. (aiōnios g166)
Paja Dema anandisiya chifukwa chokonda dziko lapansi lino, ndipo anapita ku Tesalonika. Kresike anapita ku Galatiya ndipo Tito anapita ku Dalimatiya. (aiōn g165)
căci Demas m-a părăsit, iubind lumea de acum, și s-a dus la Tesalonic, Crescens în Galatia și Tit în Dalmația. (aiōn g165)
Ambuye adzandilanditsa ku chilichonse chofuna kundichita choyipa ndipo adzandisamalira bwino mpaka kundilowetsa chonse mu ufumu wake wakumwamba. Kwa Iye kukhale ulemerero mpaka muyaya. (aiōn g165)
Și Domnul mă va izbăvi de orice lucrare rea și mă va păstra pentru Împărăția Sa cerească. A lui să fie gloria în vecii vecilor. Amin. (aiōn g165)
ndi kuwapatsa chiyembekezo cha moyo wosatha, umene Mulungu amene sanama, analonjeza nthawi isanayambe. (aiōnios g166)
în speranța vieții veșnice, pe care Dumnezeu, care nu poate minți, a făgăduit-o înainte de începutul veacurilor, (aiōnios g166)
Chisomo chimatiphunzitsa kukana moyo osalemekeza Mulungu komanso zilakolako za dziko lapansi. Ndipo chimatiphunzitsa kukhala moyo odziletsa, olungama ndi opembedza Mulungu nthawi ino, (aiōn g165)
instruindu-ne pentru ca, lepădându-ne de impietate și de poftele lumești, să trăim sobru, drept și evlavios în veacul acesta; (aiōn g165)
kuti titalungamitsidwa mwachisomo chake, tikhale olowamʼmalo okhala ndi chiyembekezo cha moyo wosatha. (aiōnios g166)
pentru ca, fiind îndreptățiți prin harul său, să fim făcuți moștenitori, potrivit cu speranța vieții veșnice. (aiōnios g166)
Mwina chifukwa chimene unasiyana naye kwa kanthawi ndi chakuti ukhale nayenso nthawi zonse. (aiōnios g166)
De aceea, poate că a fost despărțit de voi pentru o vreme, pentru ca voi să-l aveți pentru totdeauna, (aiōnios g166)
Koma masiku otsiriza ano, Mulungu wayankhula nafe kudzera mwa Mwana wake. Mwanayu anamusankha kuti akhale mwini wa zinthu zonse, ndiponso Mulungu analenga dziko lonse kudzera mwa Iye. (aiōn g165)
la sfârșitul acestor zile, ne-a vorbit prin Fiul Său, pe care L-a pus moștenitor al tuturor lucrurilor și prin care a făcut și lumile. (aiōn g165)
Koma za Mwana wake akuti, “Inu Mulungu, mpando wanu waufumu udzakhala mpaka muyaya, ndipo mudzaweruza molungama mu ufumu wanu. (aiōn g165)
Dar despre Fiul spune, “Tronul Tău, Dumnezeule, este în vecii vecilor. Sceptrul dreptății este sceptrul Împărăției Tale. (aiōn g165)
Ndipo penanso anati, “Iwe ndiwe wansembe mpaka muyaya, monga mwa unsembe wa Melikizedeki.” (aiōn g165)
După cum spune și în alt loc, “Ești preot pentru totdeauna, după ordinul lui Melchisedec.” (aiōn g165)
Atasanduka wangwiro kotheratu, anakhala gwero la chipulumutso chosatha kwa onse omvera Iye. (aiōnios g166)
Fiind desăvârșit, el a devenit pentru toți cei care îl ascultă autorul mântuirii veșnice, (aiōnios g166)
za maubatizo, za kusanjika manja, za kuuka kwa akufa ndi za chiweruzo chotsiriza. (aiōnios g166)
a învățăturii despre botezuri, despre punerea mâinilor, despre învierea morților și despre judecata veșnică. (aiōnios g166)
Analawa kukoma kwa mawu a Mulungu ndi mphamvu za nthawi ikubwera. (aiōn g165)
și au gustat cuvântul bun al lui Dumnezeu și puterile veacului viitor, (aiōn g165)
Yesu anatitsogolera kupita kumeneko, nalowako mʼmalo mwathu. Iye anasanduka Mkulu wa ansembe onse wamuyaya, monga mwa dongosolo la unsembe wa Melikizedeki. (aiōn g165)
unde, ca un precursor, Isus a intrat pentru noi, devenind Mare Preot pentru totdeauna, după rânduiala lui Melchisedec. (aiōn g165)
Pakuti Mulungu anamuchitira umboni kuti, “Iwe ndi wansembe wamuyaya, monga mwa dongosolo la unsembe wa Melikizedeki.” (aiōn g165)
căci este mărturisit, “Ești preot pentru totdeauna, conform ordinului lui Melchisedec.” (aiōn g165)
Koma Yesu ankakhala wansembe ndi lumbiro pamene Mulungu anati, “Ambuye analumbira ndipo sangasinthe maganizo ake, ‘Iwe ndi wansembe wamuyaya.’” (aiōn g165)
(căci, într-adevăr, au fost făcuți preoți fără jurământ), ci el cu jurământ, prin cel care spune despre el, “Domnul a jurat și nu se va răzgândi, 'Ești preot pentru totdeauna, conform ordinului lui Melchisedec.”” (aiōn g165)
Koma Yesu popeza ndi wamuyaya, unsembe wake ndi wosatha. (aiōn g165)
Dar el, pentru că trăiește veșnic, are o preoție neschimbată. (aiōn g165)
Pakuti lamulo limasankha anthu amene ndi ofowoka kukhala akulu a ansembe; koma lumbiro, lomwe linabwera pambuyo pa lamulo, linasankha Mwana, amene anapangidwa kukhala wangwiro kwamuyaya. (aiōn g165)
Căci legea numește ca mari preoți pe oameni care au slăbiciuni, dar cuvântul jurământului, care a venit după lege, numește pentru totdeauna un Fiu care a fost desăvârșit. (aiōn g165)
Iye sanalowemo ndi magazi ambuzi yayimuna, ana angʼombe amphongo, koma analowa Malo Opatulika kamodzi kokha ndi magazi ake, atatikonzera chipulumutso chosatha. (aiōnios g166)
și nici prin sângele țapilor și vițeilor, ci prin propriul sânge, a intrat o dată pentru totdeauna în Locul Sfânt, obținând răscumpărarea veșnică. (aiōnios g166)
nʼkoposa kotani magazi a Khristu, amene mwa Mzimu wamuyaya anadzipereka yekha kwa Mulungu kukhala nsembe yopanda chilema. Iye adzayeretsa chikumbumtima chathu pochotsa ntchito za imfa, kuti ife titumikire Mulungu wamoyo. (aiōnios g166)
cu cât mai mult sângele lui Cristos, care, prin Duhul etern, s-a oferit pe sine însuși fără cusur lui Dumnezeu, va curăța conștiința voastră de fapte moarte pentru a sluji Dumnezeului viu? (aiōnios g166)
Pa chifukwa chimenechi Khristu ndi mʼkhalapakati wa pangano latsopano, kuti iwo amene anayitanidwa alandire chuma chamuyaya, pakuti Iye tsopano anafa ngati dipo lomasula iwo ku machimo amene anachita ali pansi pa pangano loyamba lija. (aiōnios g166)
De aceea, el este mijlocitorul unui nou legământ, întrucât a avut loc o moarte pentru răscumpărarea fărădelegilor care au fost sub primul legământ, pentru ca cei care au fost chemați să primească promisiunea moștenirii veșnice. (aiōnios g166)
Zikanatero bwenzi Khristu atamva zowawa kambirimbiri chilengedwere cha dziko lapansi. Koma tsopano anaoneka kamodzi kokha chifukwa cha onse pa nthawi yotsiriza kuti achotse tchimo podzipereka yekha nsembe. (aiōn g165)
altfel trebuie să fi suferit adeseori de la întemeierea lumii. Dar acum, o singură dată, la sfârșitul veacurilor, el s-a arătat pentru a înlătura păcatul prin jertfa lui însuși. (aiōn g165)
Ndi chikhulupiriro timazindikira kuti dziko lapansi ndi la mmwamba zinapangidwa ndi Mawu a Mulungu, ndikuti zinthu zoonekazi zinachokera ku zinthu zosaoneka. (aiōn g165)
Prin credință înțelegem că universul a fost alcătuit prin Cuvântul lui Dumnezeu, astfel încât ceea ce se vede nu a fost făcut din lucruri vizibile. (aiōn g165)
Yesu Khristu ndi yemweyo dzulo, lero ndi kunthawi zonse. (aiōn g165)
Isus Hristos este același ieri, astăzi și în veci. (aiōn g165)
Mulungu wamtendere, amene kudzera mʼmagazi a pangano lamuyaya anaukitsa Ambuye athu Yesu kwa akufa, amene ndi Mʼbusa wamkulu, (aiōnios g166)
Și Dumnezeul păcii, care a înviat din morți pe marele păstor al oilor cu sângele unui legământ veșnic, pe Domnul nostru Isus, (aiōnios g166)
akupatseni chilichonse chabwino kuti muchite chifuniro chake ndipo Mulungu achite mwa ife, chimene chingamukomere kudzera mwa Yesu Khristu. Kwa Iye kukhale ulemerero ku nthawi zanthawi, Ameni. (aiōn g165)
să vă facă desăvârșiți în orice lucrare bună, ca să faceți voia Lui, lucrând în voi ceea ce este plăcut înaintea Lui, prin Isus Hristos, căruia I se cuvine slava în vecii vecilor. Amin. (aiōn g165)
Lilime nalonso ndi moto, dziko la zoyipa pakati pa ziwalo za thupi. Limawononga munthu yense wathunthu. Limayika zonse za moyo wake pa moto, ndipo moto wake ndi wochokera ku gehena. (Geenna g1067)
Și limba este un foc. Lumea nelegiuirii dintre mădularele noastre este limba, care spurcă tot trupul și dă foc cursului firii, și este incendiată de Gheenă. (Geenna g1067)
Popeza mwabadwanso, osati ndi mbewu imene imawonongeka, koma imene siwonongeka, ndiye kuti ndi Mawu a Mulungu amoyo ndi okhalitsa. (aiōn g165)
fiind născuți din nou, nu din sămânță coruptibilă, ci din incoruptibilă, prin cuvântul lui Dumnezeu, care trăiește și rămâne în veci. (aiōn g165)
koma mawu a Ambuye adzakhala mpaka muyaya.” Ndipo awa ndi mawu amene tinalalikira kwa inu. (aiōn g165)
dar cuvântul Domnului este veșnic.” Acesta este cuvântul de Buna Vestire care v-a fost propovăduit. (aiōn g165)
Ngati wina ayankhula, ayankhuledi mawu enieni a Mulungu. Ngati wina atumikira, atumikire ndi mphamvu imene Mulungu amapereka, kuti pa zonse Mulungu alemekezedwe mwa Yesu Khristu. Kwa Iye kukhale ulemerero ndi mphamvu mpaka muyaya, Ameni. (aiōn g165)
Dacă cineva vorbește, să fie ca și cum ar fi chiar cuvintele lui Dumnezeu. Dacă cineva slujește, să fie ca din puterea pe care o dă Dumnezeu, pentru ca în toate lucrurile să fie glorificat Dumnezeu prin Isus Hristos, căruia îi aparțin gloria și stăpânirea în vecii vecilor. Amin. (aiōn g165)
Ndipo Mulungu wachisomo chonse, amene anakuyitanani ku ulemerero wake wamuyaya mwa Khristu, mutamva zowawa pa kanthawi, adzakukonzaninso ndi kukulimbitsani pa maziko olimba. (aiōnios g166)
Dar fie ca Dumnezeul oricărui har, care v-a chemat la gloria Sa eternă prin Hristos Isus, după ce ați suferit puțin, să vă desăvârșească, să vă întărească, să vă întărească și să vă așeze. (aiōnios g166)
Kwa Iye kukhale mphamvu mpaka muyaya, Ameni. (aiōn g165)
A lui să fie gloria și puterea în vecii vecilor. Amin. (aiōn g165)
Mudzalandiridwa bwino kwambiri mu ufumu wosatha wa Ambuye ndi Mpulumutsi wathu Yesu Khristu. (aiōnios g166)
Căci astfel veți avea din belșug intrarea în Împărăția veșnică a Domnului și Mântuitorului nostru, Isus Hristos. (aiōnios g166)
Pakuti Mulungu sanalekerere angelo atachimwa paja, koma anawaponya mʼndende, nawayika mʼmaenje amdima, kuwasunga kuti adzaweruzidwe. (Tartaroō g5020)
Căci, dacă Dumnezeu nu a cruțat pe îngeri când au păcătuit, ci i-a aruncat în Tartar și i-a trimis în gropile întunericului, ca să fie rezervați pentru judecată; (Tartaroō g5020)
Koma kulani mu chisomo ndi mʼchidziwitso cha Ambuye ndi Mpulumutsi wathu Yesu Khristu. Kwa Iye kukhale ulemerero tsopano mpaka muyaya. Ameni. (aiōn g165)
Ci creșteți în harul și în cunoașterea Domnului și Mântuitorului nostru Isus Hristos. A lui să fie gloria acum și în veci. Amin. (aiōn g165)
Moyowo unaoneka, tinawuona ndipo tikuchitira umboni. Tikukulalikirani za moyo wosatha umene unali ndi Atate ndipo unaonekera kwa ife. (aiōnios g166)
(și viața a fost descoperită, și noi am văzut, și mărturisim și vă vestim viața, viața veșnică, care era la Tatăl și care ne-a fost descoperită); (aiōnios g166)
Dziko lapansi likupita pamodzi ndi zilakolako zake, koma amene amachita chifuniro cha Mulungu amakhalapo mpaka muyaya. (aiōn g165)
Lumea trece cu poftele ei, dar cel care face voia lui Dumnezeu rămâne pentru totdeauna. (aiōn g165)
Ndipo chimene anatilonjeza nʼchimenechi: moyo wosatha. (aiōnios g166)
Aceasta este făgăduința pe care ne-a promis-o: viața veșnică. (aiōnios g166)
Aliyense amene amadana ndi mʼbale wake ndi wakupha, ndipo inu mukudziwa kuti wopha anthu mwa iye mulibe moyo wosatha. (aiōnios g166)
Oricine își urăște fratele este un ucigaș, și știți că niciun ucigaș nu are viață veșnică rămasă în el. (aiōnios g166)
Ndipo umboniwo ndi uwu: Mulungu anatipatsa moyo wosatha, ndipo moyowu uli mwa Mwana wake. (aiōnios g166)
Mărturia este aceasta: Dumnezeu ne-a dat viața veșnică, iar această viață este în Fiul său. (aiōnios g166)
Ine ndikulemba zimenezi kwa inu, amene mwakhulupirira dzina la Mwana wa Mulungu kuti mudziwe kuti muli ndi moyo wosatha. (aiōnios g166)
Am scris aceste lucruri pentru voi, care credeți în Numele Fiului lui Dumnezeu, ca să știți că aveți viața veșnică și să credeți în continuare în Numele Fiului lui Dumnezeu. (aiōnios g166)
Tikudziwa kuti Mwana wa Mulungu anafika ndipo anatipatsa nzeru, kuti timudziwe Iye amene ali woona. Ndipo ife tili mwa Iye amene ndi woona, Mwana wake, Yesu Khristu. Iye ndi Mulungu woona ndi moyo wosatha. (aiōnios g166)
Știm că Fiul lui Dumnezeu a venit și ne-a dat pricepere, ca să cunoaștem pe cel adevărat; și noi suntem în cel adevărat, în Fiul său Isus Hristos. Acesta este adevăratul Dumnezeu și viața veșnică. (aiōnios g166)
Timakukondani chifukwa cha choonadi chimene chimakhala mwa ife ndipo chidzakhala mwa ife mpaka muyaya. (aiōn g165)
pentru adevărul care rămâne în noi și care va fi cu noi în veci: (aiōn g165)
Ndipo mukumbukire angelo amene sanakhutire ndi maudindo awo, koma anasiya malo awo. Angelo amenewa Mulungu anawamanga ndi maunyolo osatha, ndipo akuwasunga mʼmalo a mdima mpaka tsiku lalikulu lachiweruzo. (aïdios g126)
Pe îngerii care nu și-au păstrat primul domeniu, ci și-au părăsit propria locuință, i-a ținut în legături veșnice, sub întuneric, pentru judecata din ziua cea mare. (aïdios g126)
Musayiwale mizinda ya Sodomu ndi Gomora ija, ndi mizinda yoyandikana nayo. Anthu mʼmenemo anadziperekanso kuchita zadama ndi kuchita zonyansa zachilendo. Mizinda imeneyi yakhala ngati chitsanzo cha amene adzalangidwa ndi moto wosatha. (aiōnios g166)
La fel ca Sodoma și Gomora și orașele din jurul lor, care, la fel ca acestea, s-au dedat la imoralitate sexuală și au umblat după trupuri străine, sunt arătate ca exemplu, suferind pedeapsa focului veșnic. (aiōnios g166)
Iwowa ali ngati mafunde awukali apanyanja, amene amatulutsa thovu la zonyansa zawo. Amenewa ali ngati nyenyezi zosochera, ndipo Mulungu akuwasungira mdima wandiweyani mpaka muyaya. (aiōn g165)
valuri sălbatice ale mării, care își scot spuma rușinii lor; stele rătăcitoare, cărora le-a fost rezervată pentru totdeauna negura întunericului. (aiōn g165)
Khalani mʼchikondi cha Mulungu pamene mukudikira chifundo cha Ambuye athu Yesu Khristu kuti akubweretsereni moyo wosatha. (aiōnios g166)
Păstrați-vă în dragostea lui Dumnezeu, așteptând îndurarea Domnului nostru Isus Hristos pentru viața veșnică. (aiōnios g166)
kwa Mulungu yekhayo, Mpulumutsi wathu, kwa Iye kukhale ulemerero, ukulu, mphamvu ndi ulamuliro, mwa Yesu Khristu Ambuye athu, kuyambira isanayambe nthawi, tsopano mpaka muyaya. Ameni. (aiōn g165)
lui Dumnezeu, Mântuitorul nostru, singurul înțelept, fie slava și maiestatea, stăpânirea și puterea, acum și pururea și în vecii vecilor. Amin. (aiōn g165)
ndipo watisandutsa mafumu ndi ansembe kuti tizitumikira Mulungu ndi Atate ake. Kwa Iye kukhale ulemerero ndi mphamvu ku nthawi zosatha, Ameni. (aiōn g165)
și ne-a făcut să fim un regat, preoți ai Dumnezeului și Tatălui său — lui să fie gloria și stăpânirea în vecii vecilor. Amin. (aiōn g165)
Ine ndine Wamoyo; ndinali wakufa ndipo taona ndine wamoyo mpaka muyaya! Ndipo ndili ndi makiyi a imfa ndi Hade. (aiōn g165, Hadēs g86)
și Cel viu. Am fost mort și iată că sunt viu în vecii vecilor. Amin. Eu am cheile Morții și ale Hadesului. (aiōn g165, Hadēs g86)
Nthawi zonse zamoyozo zimapereka ulemerero, ulemu ndi mayamiko kwa uja wokhala pa mpando waufumu, amene ali ndi moyo wamuyaya. (aiōn g165)
Când făpturile vii vor da slavă, cinste și mulțumire Celui ce șade pe tron, Celui ce trăiește în vecii vecilor, (aiōn g165)
Izi zikamachitika akuluakulu 24 aja amadzigwetsa pansi pamaso pa wokhala pa mpando waufumuyo, namupembedza wokhala ndi moyo wamuyayayo. Iwo amaponya pansi zipewa zawo zaufumu patsogolo pa mpando waufumu nati: (aiōn g165)
cei douăzeci și patru de bătrâni se vor arunca înaintea Celui ce șade pe tron și se vor închina Celui ce trăiește în vecii vecilor și își vor arunca coroanele înaintea tronului, zicând: (aiōn g165)
Kenaka ndinamva mawu a cholengedwa chilichonse kumwamba, pa dziko lapansi, kunsi kwa dziko lapansi, pa nyanja ndi zonse zili mʼmenemo zikuyimba kuti, “Kwa wokhala pa mpando waufumu ndi kwa Mwana Wankhosa, kukhale mayamiko, ulemu, ulemerero ndi mphamvu (aiōn g165)
Și am auzit toate făpturile care sunt în ceruri, pe pământ, sub pământ, pe mare și tot ce este în ele, zicând: “Binecuvântarea, cinstea, slava și stăpânirea să fie pentru Cel ce șade pe scaunul de domnie și pentru Miel, în vecii vecilor! Amin!” (aiōn g165)
Nditayangʼana patsogolo panga ndinaona kavalo wotuwa! Wokwerapo wake dzina lake linali Imfa ndipo Hade inali kumutsatira pambuyo pake. Anapatsidwa ulamuliro pa gawo limodzi la magawo anayi a dziko lapansi kuti aphe ndi lupanga, njala, mliri, ndi zirombo zakuthengo za mʼdziko lapansi. (Hadēs g86)
Și iată un cal palid, iar numele celui care ședea pe el era Moartea. Hades îl urma cu el. I s-a dat autoritate asupra unui sfert din pământ, ca să ucidă cu sabia, cu foametea, cu moartea și cu animalele sălbatice de pe pământ. (Hadēs g86)
Iwo anati, “Ameni! Matamando ndi ulemerero, nzeru, mayamiko, ulemu, ulamuliro ndi mphamvu zikhale kwa Mulungu wathu kunthawi zanthawi, Ameni!” (aiōn g165)
zicând: “Amin! Binecuvântare, glorie, înțelepciune, mulțumire, onoare, putere și tărie să fie pentru Dumnezeul nostru în vecii vecilor! Amin.” (aiōn g165)
Mngelo wachisanu anayimba lipenga lake, ndipo ndinaona nyenyezi ikugwa pa dziko lapansi kuchokera ku thambo. Nyenyeziyo inapatsidwa kiyi ya ku chidzenje chakuya. (Abyssos g12)
Îngerul al cincilea a sunat din glas și am văzut din cer o stea care a căzut pe pământ. Cheia de la groapa abisului i-a fost dată. (Abyssos g12)
Nyenyeziyo itatsekula pa chidzenje chakuyacho panatuluka utsi ngati wochokera mʼngʼanjo yayikulu. Dzuwa ndi thambo zinada chifukwa cha utsi ochokera mʼdzenjemo. (Abyssos g12)
El a deschis groapa abisului și din groapă a ieșit fum ca fumul unui cuptor aprins. Soarele și aerul s-au întunecat din cauza fumului care ieșea din groapă. (Abyssos g12)
Mfumu yawo inali mngelo wolamulira Chidzenje chakuya chija. Mʼchihebri dzina lake ndi Abadoni ndipo mʼChigriki ndi Apoliyoni (tanthauzo lake ndiye kuti, Wowononga). (Abyssos g12)
Ei au peste ei ca rege pe îngerul abisului. Numele lui în ebraică este “Abaddon”, dar în greacă are numele “Apollyon”. (Abyssos g12)
Mngeloyo analumbira mʼdzina la Iye wokhala ndi moyo mpaka muyaya, amene analenga kumwamba ndi zonse zili kumeneko, dziko lapansi ndi zonse zili mʼmenemo, nyanja ndi zonse zili mʼmenemo, nati, “Pasakhalenso zochedwa tsopano! (aiōn g165)
și a jurat pe Cel ce trăiește în vecii vecilor, care a creat cerul și lucrurile care sunt în el, pământul și lucrurile care sunt în el, marea și lucrurile care sunt în ea, că nu va mai fi nici o întârziere, (aiōn g165)
Tsono zikadzatsiriza umboni wawowo, chirombo chotuluka mʼChidzenje chakuya chija chidzachita nawo nkhondo nʼkuzigonjetsa mpaka kuzipha. (Abyssos g12)
După ce-și vor fi isprăvit mărturia lor, fiara care se va ridica din prăpastie va face război cu ei, îi va birui și-i va ucide. (Abyssos g12)
Mngelo wachisanu ndi chiwiri anawomba lipenga lake, ndipo kumwamba kunamveka mawu ofuwula amene anati, “Ufumu wa dziko lapansi uli mʼmanja mwa Ambuye athu ndi Khristu wake uja, ndipo adzalamulira mpaka muyaya.” (aiōn g165)
Îngerul al șaptelea a sunat și au urmat glasuri mari în ceruri, care ziceau: “Împărăția lumii a devenit Împărăția Domnului nostru și a Hristosului Său. El va domni în vecii vecilor!” (aiōn g165)
Kenaka ndinaona mngelo wina akuwuluka mu mlengalenga ndipo anali ndi Uthenga Wabwino wamuyaya woti akalalikire kwa anthu okhala pa dziko lapansi, kwa a mtundu uliwonse, a fuko lililonse, a chiyankhulo chilichonse ndi kwa anthu onse. (aiōnios g166)
Și am văzut un înger care zbura din mijlocul cerului și care avea o veste veșnică, pe care trebuia să o vestească celor ce locuiesc pe pământ, oricărui neam, seminție, limbă și popor. (aiōnios g166)
Ndipo utsi wa moto wowazunzawo udzakwera kumwamba mpaka muyaya. Sikudzakhala kupumula usana ndi usiku kwa amene anapembedza chirombo chija ndi fano lake kapena kwa aliyense amene analembedwa chizindikiro cha dzina lake lija.” (aiōn g165)
Fumul chinului lor se va ridica în vecii vecilor. Nu au odihnă zi și noapte, cei care se închină fiarei și chipului ei și oricine primește semnul numelui ei. (aiōn g165)
Ndipo kenaka chimodzi cha zamoyo zinayi zija chinapereka kwa angelo asanu ndi awiri mbale zisanu ndi ziwiri zodzaza ndi ukali wa Mulungu amene ali ndi moyo mpaka muyaya. (aiōn g165)
Una din cele patru făpturi vii a dat celor șapte îngeri șapte cupe de aur pline cu mânia lui Dumnezeu, care trăiește în vecii vecilor. (aiōn g165)
Chirombo chimene wachionachi chinalipo kale koma tsopano kulibe ndipo chidzatuluka ku chidzenje chakuya ndi kupita kukawonongedwa. Anthu okhala pa dziko lapansi amene mayina awo sanalembedwe mʼbuku lamoyo kuyambira pa kulengedwa kwa dziko lapansi adzadabwa pamene adzaona chirombocho, chifukwa chinalipo kale, tsopano kulibe, komabe chidzabwera. (Abyssos g12)
Fiara pe care ai văzut-o a fost și nu mai este; și este pe cale să iasă din abis și să meargă la pieire. Cei care locuiesc pe pământ și ale căror nume nu au fost scrise în cartea vieții de la întemeierea lumii se vor minuna când vor vedea că fiara a fost și nu este, și va fi prezentă. (Abyssos g12)
Ndipo anafuwulanso kuti, “Haleluya! Utsi wochokera kwa mkazi wadamayo udzakwera kumwamba mpaka muyaya.” (aiōn g165)
Al doilea a zis: “Aleluia! Fumul ei se ridică în vecii vecilor”. (aiōn g165)
Koma chirombocho chinagwidwa pamodzi ndi mneneri wonyenga uja amene anachita zizindikiro zodabwitsa pamaso pake. Ndi zizindikirozi anasocheretsa amene analembedwa chizindikiro cha chirombocho napembedza fano lake. Onse awiri anaponyedwa amoyo mʼnyanja yamoto yasulufule wotentha. (Limnē Pyr g3041 g4442)
Fiara a fost prinsă și, împreună cu ea, falsul profet care făcea semnele pe care le făcea în fața lui, prin care îi înșela pe cei care primiseră semnul fiarei și pe cei care se închinau chipului ei. Aceștia doi au fost aruncați de vii în lacul de foc care arde cu sulf. (Limnē Pyr g3041 g4442)
Ndipo ndinaona mngelo akutsika kuchokera kumwamba ali ndi kiyi ya ku chidzenje chakuya chija atanyamula mʼdzanja lake unyolo waukulu. (Abyssos g12)
Am văzut un înger coborând din cer, având în mână cheia prăpastiei și un lanț mare. (Abyssos g12)
Anamuponya ku chidzenje chakuya chija namutsekera ndi kiyi ndi kumatirira pa khomopo kuti asatulukenso kukanyenga mitundu ya anthu mpaka patapita zaka 1,000. Zikadzatha zakazo, adzamumasula kwa kanthawi pangʼono chabe. (Abyssos g12)
l-a aruncat în abis, l-a închis și l-a pecetluit peste el, ca să nu mai înșele neamurile până la sfârșitul celor o mie de ani. După aceasta, el trebuie să fie eliberat pentru o scurtă perioadă de timp. (Abyssos g12)
Ndipo Mdierekezi amene anawanyenga, anaponyedwa mʼnyanja ya sulufule wotentha, kumene kunaponyedwa chirombo chija ndi mneneri wonama uja. Iwo adzazunzika usiku ndi usana kwamuyaya. (aiōn g165, Limnē Pyr g3041 g4442)
Diavolul care i-a înșelat a fost aruncat în iazul de foc și de sulf, unde sunt și fiara și falsul profet. Ei vor fi chinuiți zi și noapte în vecii vecilor. (aiōn g165, Limnē Pyr g3041 g4442)
Nyanja inapereka amene anaferamo ndipo imfa ndi Hade zinapereka akufa ake ndipo munthu aliyense anaweruzidwa monga mwa ntchito zake. (Hadēs g86)
Marea a dat pe față morții care se aflau în ea. Moartea și Hadesul au renunțat la morții care erau în ele. Au fost judecați, fiecare după faptele sale. (Hadēs g86)
Kenaka imfa ndi Hade zinaponyedwa mʼnyanja ya moto. Nyanja yamoto ndiyo imfa yachiwiri. (Hadēs g86, Limnē Pyr g3041 g4442)
Moartea și Hadesul au fost aruncate în lacul de foc. Aceasta este a doua moarte, lacul de foc. (Hadēs g86, Limnē Pyr g3041 g4442)
Ngati dzina la wina aliyense silinapezeke mʼBuku Lamoyo, anaponyedwa mʼnyanja yamoto. (Limnē Pyr g3041 g4442)
Dacă cineva nu era găsit scris în cartea vieții, era aruncat în lacul de foc. (Limnē Pyr g3041 g4442)
Koma amantha, osakhulupirira, okonda zonyansa, opha anthu, achiwerewere, amatsenga, opembedza mafano ndi abodza, malo awo adzakhala nyanja yamoto ya sulufule wotentha. Iyi ndi imfa yachiwiri.” (Limnē Pyr g3041 g4442)
Dar pentru cei lași, necredincioși, păcătoși, abominabili, ucigași, imorali, vrăjitori, închinători la idoli și toți mincinoșii, partea lor este în lacul care arde cu foc și sulf, care este moartea a doua.” (Limnē Pyr g3041 g4442)
Sipadzakhalanso usiku. Sadzafuna kuwala kwa nyale kapena kwa dzuwa pakuti Ambuye Mulungu adzakhala kuwala kwawo. Ndipo adzalamulira kwamuyaya. (aiōn g165)
Nu va mai fi noapte și nu vor avea nevoie de lumina lămpii sau de lumina soarelui, pentru că Domnul Dumnezeu îi va lumina. Ei vor domni în vecii vecilor. (aiōn g165)

CHW > Aionian Verses: 264
RFB > Aionian Verses: 200