Aionian Verses
Ngakhale kuti ana ake onse aamuna ndi aakazi anasonkhana kudzamutonthoza, iye anakana kutonthozedwa. Iye anati, “Ayi. Ndidzalira mpaka ndidzapite kwa mwana wanga ku manda.” Choncho Israeli anapitirirabe kulira mwana wake. (Sheol )
(parallel missing)
Koma Yakobo anati, “Mwana wanga sapita nanu kumeneko; mkulu wake anamwalira ndipo watsala yekha. Ngati choyipa chitamuchitikira pa ulendo mukupitawu, ndiye kuti ndi mmene ndakalambiramu inu mudzandipha ndi chisoni chotere.” (Sheol )
(parallel missing)
Tsopano mukanditengeranso uyu, nakaphedwa mu njira ndiye kuti mudzandikankhira ku manda ndi chisoni.’ (Sheol )
(parallel missing)
ndipo akakaona kuti mnyamatayu palibe, basi akafa. Ife tidzakhala ngati takankhira abambo athu ku manda ndi chisoni. (Sheol )
(parallel missing)
Koma Yehova akachita china chake chachilendo, nthaka nitsekula pakamwa pake ndi kuwameza iwo pamodzi ndi zonse zimene ali nazo, iwowa nʼkulowa mʼmanda ali moyo, pamenepo mudzazindikira kuti anthu amenewa ananyoza Yehova.” (Sheol )
(parallel missing)
Analowa mʼmanda amoyo pamodzi ndi zonse zimene anali nazo. Nthaka inawatsekera ndi kuwawononga ndipo sanaonekenso. (Sheol )
(parallel missing)
Pakuti mkwiyo wanga wayaka ngati moto, umene umayaka mpaka ku dziko la anthu akufa. Motowo udzanyeketsa dziko lapansi ndi zokolola zake ndipo udzapsereza maziko a mapiri. (Sheol )
(parallel missing)
“Yehova amabweretsa imfa ndipo amaperekanso moyo, amatsitsira ku manda ndipo amawatulutsakonso. (Sheol )
(parallel missing)
Anandimanga ndi zingwe za ku manda; misampha ya imfa inalimbana nane. (Sheol )
(parallel missing)
Iwe uchite kwa iye molingana ndi nzeru zako, koma usalole kuti afe ndi ukalamba ndi kupita ku manda mwamtendere. (Sheol )
(parallel missing)
Koma tsopano usamuyese ngati munthu wosalakwa. Iwe ndiwe munthu wanzeru. Udzadziwa choti uchite naye. Ngakhale ndi wokalamba, aphedwe ndithu.” (Sheol )
(parallel missing)
Monga mtambo umazimirira ndi kukanganuka, momwemonso munthu amene walowa mʼmanda sabwerera. (Sheol )
(parallel missing)
Zili kutali kupambana mayiko akumwamba, nanga ungachite chiyani? Ndi zakuya kupambana kuya kwa manda, nanga ungadziwe chiyani? (Sheol )
(parallel missing)
“Aa, Inu mukanangondibisa mʼmanda ndi kundiphimba kuti ndisaoneke mpaka mkwiyo wanu utapita! Achikhala munandiyikira nthawi, kuti pambuyo pake mundikumbukirenso. (Sheol )
(parallel missing)
Ngati nyumba imene ndikuyiyembekezera ndi manda, ngati ndiyala bedi langa mu mdima, (Sheol )
(parallel missing)
Ndithu sindidzakhalanso ndi chiyembekezo chilichonse, polowa mʼmanda, pamene ndidzatsikira ku fumbi.” (Sheol )
(parallel missing)
Zaka zawo zimatha ali mu ulemerero ndipo amatsikira ku manda mwamtendere. (Sheol )
(parallel missing)
Monga momwe kutentha ndi chilala zimasungunulira madzi owundana ndi momwemonso mmene manda amachotsera omwe achimwa. (Sheol )
(parallel missing)
Dziko la anthu akufa ndi lapululu pamaso pa Mulungu; chiwonongeko ndi chosaphimbidwa. (Sheol )
(parallel missing)
Palibe amene amakukumbukirani pamene wamwalira; Amakutamandani ndani ali ku manda? (Sheol )
(parallel missing)
Oyipa amabwerera ku manda, mitundu yonse imene imayiwala Mulungu. (Sheol )
(parallel missing)
chifukwa Inu simudzandisiya ku manda, simudzalola kuti woyera wanu avunde. (Sheol )
(parallel missing)
Anandimanga ndi zingwe za ku manda; misampha ya imfa inalimbana nane. (Sheol )
(parallel missing)
Inu Yehova, munanditulutsa ku manda, munandisunga kuti ndisatsalire mʼdzenje. (Sheol )
(parallel missing)
Yehova musalole kuti ndichite manyazi, pakuti ndalirira kwa Inu; koma oyipa achititsidwe manyazi ndipo agone chete mʼmanda. (Sheol )
(parallel missing)
Monga nkhosa iwo ayenera kupita ku manda, ndipo imfa idzawadya. Olungama adzawalamulira mmawa; matupi awo adzavunda mʼmanda, kutali ndi nyumba zawo zaufumu. (Sheol )
(parallel missing)
Koma Mulungu adzawombola moyo wanga kuchoka ku manda; ndithu Iye adzanditengera kwa Iye mwini. (Sheol )
(parallel missing)
Mulole imfa itenge adani anga mwadzidzidzi; alowe mʼmanda ali amoyo pakuti choyipa chili pakati pawo. (Sheol )
(parallel missing)
Pakuti chikondi chanu nʼchachikulu kwa ine; mwandipulumutsa ku malo ozama a manda. (Sheol )
(parallel missing)
Pakuti ndili ndi mavuto ambiri ndipo moyo wanga ukuyandikira ku manda. (Sheol )
(parallel missing)
Kodi ndi munthu uti angakhale ndi moyo ndi kusaona imfa? Kapena kudzipulumutsa yekha ku mphamvu ya manda? (Sela) (Sheol )
(parallel missing)
Zingwe za imfa zinandizinga, zoopsa za ku dziko la anthu akufa zinandigwera; ndinapeza mavuto ndi chisoni. (Sheol )
(parallel missing)
Ndikakwera kumwamba, Inu muli komweko; ndikakagona ku malo a anthu akufa, Inu muli komweko. (Sheol )
(parallel missing)
Iwo adzati, “Monga momwe nkhuni zimamwazikira akaziwaza, ndi momwenso mafupa athu amwazikira pa khomo la manda.” (Sheol )
(parallel missing)
tiwameze amoyo ngati manda, ndi athunthu ngati anthu otsikira mʼdzenje. (Sheol )
(parallel missing)
Mapazi ake amatsikira ku imfa; akamayenda ndiye kuti akupita ku manda. (Sheol )
(parallel missing)
Nyumba yake ndi njira yopita ku manda, yotsikira ku malo a anthu akufa. (Sheol )
(parallel missing)
Koma amunawo sadziwa kuti akufa ali kale komweko, ndi kuti alendo ake alowa kale mʼmanda akuya. (Sheol )
(parallel missing)
Manda ndi chiwonongeko ndi zosabisika pamaso pa Yehova, nanji mitima ya anthu! (Sheol )
(parallel missing)
Munthu wanzeru amatsata njira yopita ku moyo kuti apewe malo okhala anthu akufa. (Sheol )
(parallel missing)
Ukamukwapula ndi tsatsa udzapulumutsa moyo wake. (Sheol )
(parallel missing)
Manda sakhuta, nawonso maso a munthu sakhuta. (Sheol )
(parallel missing)
Manda, mkazi wosabala, nthaka yosakhuta madzi ndiponso moto womangoyakirayakira!” (Sheol )
(parallel missing)
Ntchito iliyonse imene ukuyigwira, uyigwire ndi mphamvu zako zonse, pakuti ku manda kumene ukupita kulibe kugwira ntchito, kulibe malingaliro, chidziwitso ndiponso nzeru. (Sheol )
(parallel missing)
Undiyike pamtima pako ngati chidindo, ngati chidindo cha pa dzanja lako; pakuti chikondi nʼchamphamvu ngati imfa, nsanje ndiyaliwuma ngati manda. Chikondi chimachita kuti lawilawi ngati malawi a moto wamphamvu. (Sheol )
(parallel missing)
Nʼchifukwa chake ku manda sikukhuta ndipo kwayasama kwambiri kukamwa kwake; mʼmandamo mudzagweranso anthu otchuka a mu Yerusalemu pamodzi ndi anthu wamba ochuluka; adzagweramo ali wowowo, nʼkuledzera kwawoko. (Sheol )
(parallel missing)
“Pempha chizindikiro kwa Yehova Mulungu wako, chikhale chozama ngati manda kapena chachitali ngati mlengalenga.” (Sheol )
(parallel missing)
Ku manda kwatekeseka kuti akulandire ukamabwera; mizimu ya anthu akufa, aja amene anali atsogoleri a dziko lapansi, yadzutsidwa. Onse amene anali mafumu a mitundu ya anthu ayimiritsidwa pa mipando yawo. (Sheol )
(parallel missing)
Ulemerero wako wonse walowa mʼmanda, pamodzi ndi nyimbo za azeze ako; mphutsi zayalana pogona pako ndipo chofunda chako ndi nyongolotsi. (Sheol )
(parallel missing)
Koma watsitsidwa mʼmanda pansi penipeni pa dzenje. (Sheol )
(parallel missing)
Inu mumayankhula monyada kuti, “Ife tinachita pangano ndi imfa, ife tachita mgwirizano ndi manda. Pamene mliri woopsa ukadzafika sudzatikhudza ife, chifukwa timadalira bodza ngati pothawirapo pathu ndi chinyengo ngati malo anthu obisalapo.” (Sheol )
(parallel missing)
Pangano limene munachita ndi imfa lidzathetsedwa; mgwirizano wanu ndi manda udzachotsedwa. Pakuti mliri woopsa udzafika, ndipo udzakugonjetsani. (Sheol )
(parallel missing)
Ine ndinaganiza kuti ndidzapita ku dziko la akufa pamene moyo ukukoma. (Sheol )
(parallel missing)
Pakuti akumanda sangathe kukutamandani, akufa sangayimbe nyimbo yokutamandani. Iwo amene akutsikira ku dzenje sangakukhulupirireni. (Sheol )
(parallel missing)
Mumapita kukapembedza fano la Moleki mutatenga mafuta ndi zonunkhira zochuluka. Munachita kutumiza akazembe anu kutali; inu ngakhale munapita ku manda kwenikweniko! (Sheol )
(parallel missing)
“‘Ine Ambuye Yehova ndikuti: Pa nthawi imene mkungudzawo unatsikira ku manda, ndinawuza nyanja kuti iwulire maliro pakuwuphimba. Ndinawumitsa mitsinje ndipo madzi ambiri anaphwa. Ndinabweretsa mdima pa Lebanoni chifukwa cha mtengowo ndipo mitengo yonse ya mʼdzikomo inawuma. (Sheol )
(parallel missing)
Mitundu ya anthu inagwedezeka pakumva mkokomo wa kugwa kwake, pamene ndinawutsitsira ku manda pamodzi ndi iwo amene anafa. Pamenepo ku dziko la akufa mitengo yonse ya ku Edeni pamodzi ndi ya ku Lebanoni yosankhidwa bwino inasangalatsidwa chifukwa cha zimenezi. (Sheol )
(parallel missing)
Amene ankakhala mu mthunzi wake, amene ankayanjana nawo, iwonso anapita nawo pamodzi ku manda, kukakhala pamodzi ndi amene anaphedwa ndi lupanga pakati pa mitundu ya anthu. (Sheol )
(parallel missing)
Mʼkati mwa manda atsogoleri amphamvu pamodzi ndi ogwirizana nawo azidzakambirana za Igupto nʼkumati, ‘Afika kuno anthu osachita mdulidwe aja! Ndi awa agona apawa, ophedwa pa nkhondo.’ (Sheol )
(parallel missing)
Iwo sanayikidwe mwaulemu ngati ankhondo amphamvu amakedzana, amene anatsikira ku dziko la anthu akufa ndi zida zawo zomwe za nkhondo. Malupanga awo anawayika ku mitu yawo, ndipo zishango zawo anaphimba mafupa awo. Kale anthu amphamvu amenewa ankaopsa dziko la anthu amoyo. (Sheol )
(parallel missing)
“Ndidzawapulumutsa ku mphamvu ya manda; ndidzawawombola ku imfa. Kodi iwe imfa, miliri yako ili kuti? Kodi iwe manda, kuwononga kwako kuli kuti? “Sindidzachitanso chifundo, (Sheol )
(parallel missing)
Ngakhale atakumba pansi mpaka ku malo a anthu akufa, dzanja langa lidzawatulutsa kumeneko. Ngakhale atakwera kumwamba Ine ndidzawatsakamutsa kumeneko. (Sheol )
(parallel missing)
Iye anati: “Pamene ndinali mʼmavuto anga ndinayitana Yehova, ndipo Iye anandiyankha. Ndili ku dziko la anthu akufa ndinapempha thandizo, ndipo Inu munamva kulira kwanga. (Sheol )
(parallel missing)
Ndithu, wasokonezeka ndi vinyo; ndi wodzitama ndiponso wosakhazikika. Pakuti ngodzikonda ngati manda, ngosakhutitsidwa ngati imfa, wadzisonkhanitsira mitundu yonse ya anthu ndipo wagwira ukapolo anthu a mitundu yonse. (Sheol )
(parallel missing)
Koma Ine ndikukuwuzani kuti aliyense wokwiyira mʼbale wake adzapezeka wolakwa ku bwalo la milandu. Ndiponso aliyense amene wonena mʼbale wake kuti, ‘Ndiwe wopanda phindu,’ adzapezeka wolakwa ku bwalo la milandu lalikulu. Ndipo aliyense amene anganene mnzake ‘wopandapake’ adzatengeredwa ku bwalo la milandu. Ndiponso aliyense amene angamunene mnzake kuti, ‘Chitsiru iwe,’ adzaponyedwa ku gehena. (Geenna )
Adubu eina nakhoida hairibasini, kanagumba amana magi machin-manaogi mathakta saorabadi, wayen-gi awabada tagani. Aduga amuksu, kanagumbana magi machin manaoda ‘Raca’ haina hairabadi mahakna sanhedrin-gi mamangda pukhatpagi khudongthiba adu nanggani. Amasung kanagumbana mahakki machin manaoda ‘Apang mirem’ hairabadi mahakna norokki meigi awabada tagani. (Geenna )
Ngati diso lako lakumanja likuchimwitsa, ulichotse ndi kulitaya. Pakuti nʼkwabwino kwa iwe kutaya chiwalo chimodzi cha thupi lako, kusiyana ndi kuti thupi lonse liponyedwe mʼgehena. (Geenna )
Aduga karigumba nahakki yetthangba mitna nahakpu papta tahallabadi, madu kothoktuna nangondagi langthok-u; maramdi nahakki hakchang apumba norokta langsinkhigadabagi sarukpudi, nahakki hakchanggi kayat ama mangkhibana nahakkidamak henna phei. (Geenna )
Ndipo ngati dzanja lako lamanja likuchimwitsa, ulidule ndi kulitaya. Pakuti nʼkwabwino kwa iwe kutaya chiwalo chimodzi cha thupi lako, kusiyana ndi kuti thupi lonse liponyedwe mʼgehena. (Geenna )
Aduga nahakki yetthangba khutna nahakpu papta tahallabadi madu kakthattuna langthok-u; maramdi nahakki hakchang apumba norokta chatkadabagi sarukpudi, nahakki hakchang kayat ama mangkhibana nahakkidamak henna phei. (Geenna )
Musamaope amene amapha thupi koma sangathe kuchotsa moyo. Koma muziopa Iye amene akhoza kupha mzimu ndi kuwononga thupi mu gehena. (Geenna )
Aduga hakchangbu hatlaga, thawaibudi hatpa ngamdaba makhoising adubu kiganu; adubu thawai amasung hakchang animakpu norokta manghanba ngamba Ibungo mahakpu kiyu. (Geenna )
Ndipo iwe Kaperenawo, kodi udzakwezedwa kufika kumwamba? Ayi, udzatsitsidwa mpaka pansi kufika ku Hade. Ngati zodabwitsa zimene zinachitika mwa iwe, zikanachitika mu Sodomu, bwenzi iye alipo kufikira lero. (Hadēs )
Aduga he Capernaum, nangdi swargada ikai khumnaba phanggadra? Natte, nangdi khamnung leibakta kumlagani, maramdi nangonda toukhiba angakpa thabaksing adu Sodom-da touramlabadi, ngasi phaoba Sodom leiramgadabani. (Hadēs )
Aliyense amene anena mawu otsutsana ndi Mwana wa Munthu adzakhululukidwa koma aliyense wonena motsutsana ndi Mzimu Woyera sadzakhululukidwa mu mʼbado uno kapena umene ukubwerawo. (aiōn )
Aduga Migi Machanupa adugi mathakta wa ngangba mahak adubu kokpigani, adubu Thawai Asengbagi mathakta ngangba mahak adubu houjikki mirol asidasu aduga lakkadaba miroldasu kokpiroi. (aiōn )
Zimene zinafesedwa pakati pa minga, ndi munthu amene amamva mawu koma nkhawa za moyo uno ndi chinyengo cha chuma zimalepheretsa mawuwo kuti abale chipatso. (aiōn )
Aduga tingkhang marakta hunba maru aduna wa adu tariba makhoising aduni. Adubu taibangpan punsi asigi langtaknaba amadi lanthumgi oiba nungaibagi lounamna wa adubu namhatkhibana makhoina mahei yanba ngamde. (aiōn )
Ndipo amene anafesa namsongole ndi Satana. Kukolola ndiko kutha kwa dzikoli ndipo otuta ndi angelo. (aiōn )
Amasung makhoising adubu hullamba yeknaba aduna Devil-ni. Lokpagi matam aduna taibangpangi aroiba matam aduni, aduga lokpagi thabak suribasing aduna swargadutnisingni. (aiōn )
“Monga momwe namsongole azulidwa ndi kutenthedwa ndi moto, momwemonso kudzakhala pakutha kwa dziko. (aiōn )
Aduga napising adubu khomjillaga meida thajinba aduga chap mannana taibangpangi aroiba matam adudasu oigani. (aiōn )
Umu ndi mmene kudzakhalira pakutha kwa dziko. Angelo adzabwera ndi kulekanitsa oyipa ndi olungama. (aiōn )
Aduga taibangpangi aroiba matam adudasu matou asumna oigani. Swargadutsingna laktuna achumba chatpasingdagi phattaba misingbu tonganna khaidokkani. (aiōn )
Ndipo Ine ndikuwuza iwe kuti ndiwe Petro ndipo pa thanthwe ili Ine ndidzamangapo mpingo wanga ndipo makomo a ku gehena sadzawugonjetsa. (Hadēs )
Aduga eina nangonda hairi, madudi nahakti Peter-ni, nungjao asigi mathakta eina eigi singlup sagani, aduga khamnung leibakki panggalna madubu maithiba piba ngamloi. (Hadēs )
Ngati dzanja lako kapena phazi lako likuchimwitsa, lidule ndi kulitaya. Ndi bwino kwa iwe kulowa mʼmoyo wosatha wolumala kusiyana ndi kukhala ndi manja awiri kapena mapazi awiri ndi kukaponyedwa ku moto wosatha. (aiōnios )
“Aduga nahakki nakhut nattraga nakhongna nahakpu papta tahallabadi, madu kakthattuna langthokkho. Maramdi nakhut ani amadi nakhong ani pallaga lomba naidaba meinungda langsinbabudi, nakhut soinaina amadi khong tekna hingbada changbana nahakidamak henna phei. (aiōnios )
Ndipo ngati diso lako likuchimwitsa, ulichotse ndi kulitaya. Ndi bwino kwa iwe kuti ukalowe ku moyo wosatha ndi diso limodzi kuposa ndi kukhala ndi maso awiri ndi kukaponyedwa ku moto wa gehena.” (Geenna )
Aduga nahakki mitna nahakpu papta tahallabadi, madu kotthoktuna langthokkho. Maramdi namit ani pallaga norokki meinungda langsinbabudi, namit namatang pallaga hingbada changbana nahakkidamak henna phei. (Geenna )
Taonani mnyamata wina anabwera kwa Yesu namufunsa kuti, “Aphunzitsi, ndi chinthu chiti chabwino chimene ndiyenera kuchita kuti ndipeze moyo wosatha?” (aiōnios )
Nongma nupa amana Jisugi nakta laktuna asumna hangjarammi, “Aphaba Oja Ibungo, lomba naidaba hingba phangnanaba eina kari aphaba thabak toujagadage?” (aiōnios )
Ndipo aliyense amene wasiya nyumba, kapena abale, kapena alongo, kapena bambo kapena mayi kapena mkazi, kapena ana, kapena minda chifukwa cha Ine adzalandira madalitso ochuluka ndi kulandiranso moyo wosatha. (aiōnios )
Aduga eigi maramgidamak mayum makei, machin-manao, machan-mache, mama mapa, macha-masu, lou-sing thadokpa mi khudingmakna madugi saruk chama henna amasung lomba naidaba hingba phangjagani. (aiōnios )
Ataona mtengo wamkuyu mʼmbali mwa msewu, anapitapo koma sanapeze kanthu koma masamba okhaokha. Pamenepo anati kwa mtengowo, “Usadzabalenso chipatso!” Nthawi yomweyo mtengowo unafota. (aiōn )
Aduga Ibungona lambi mapanda heiyit pambi ama houba ubada pambidugi manakta changlammi adubu manakhak nattana mahei amata panba thengnaramde. Maduda Ibungona heiyit pambi aduda hairak-i, “Matam pumnamakta nahak mahei pandaba oirasanu!” Aduga khudak aduda heiyit pambi adu kangsillaklammi. (aiōn )
“Tsoka kwa inu, aphunzitsi amalamulo ndi Afarisi, achiphamaso! Mumayenda maulendo ambiri pa mtunda ndi pa nyanja kuti mutembenuze munthu mmodzi, ndipo akatembenuka, mumamusandutsa kukhala mwana wa gehena kawiri kuposa inu. (Geenna )
“Aphasasinaba, he Wayel Yathanggi ojasing amasung Pharisee-sing nakhoidi awabanida! Maramdi nakhoina mi amabu nakhoigi lainingda olhannabagidamak ipak kaya amasung lamdam kaya koina chatli. Aduga mahakna ollaklabada mahakpu nakhoina oiba adudagi saruk ani henna norokki macha oihalli.” (Geenna )
“Njoka inu! Ana amamba! Mudzachithawa bwanji chilango cha gehena? (Geenna )
He lilsa, he lindugi machasa, norokki wayen adudagi nakhoina karamna nanthokkadage? (Geenna )
Pamene Yesu anakhala pansi pa phiri la Olivi, ophunzira ake anabwera kwa Iye mwamseri nati, “Tiwuzeni, kodi izi zidzachitika liti, ndipo chizindikiro cha kubwera kwanu ndi zizindikiro za kutha kwa dziko zidzakhala chiyani?” (aiōn )
Aduga Jisuna chorphon chingthakta phamlingeida tung-inbasing aduna Ibungogi nakta makhoi khaktamak lakladuna hairak-i, “Pumnamaksing asi karamba matamda thokkadage? Ibungona amuk lengbirakkadaba amasung taibangpan-gi aroiba matamgi khudam adu karino haiba eikhoida takpiyu.” (aiōn )
“Pamenepo adzanena kwa akumanzere kwake kuti, ‘Chokani kwa Ine, inu otembereredwa, pitani ku moto wosatha wokonzedwera mdierekezi ndi angelo ake. (aiōnios )
“Adudagi Ibungona mahakki oiromda leibasing aduda haigani, ‘He sirap phangbasa, eingondagi chatthoktuna Satan amasung mahakki dutsingidamak thourang toukhraba mutpa naidaba mei aduda chatkhro! (aiōnios )
“Amenewa adzapita ku chilango chosatha pamene olungama ku moyo wosatha.” (aiōnios )
Adudagi makhoina lomba naidaba cheirak phanggadaba maphamda chatkani, adubu achumba chatpasingna lomba naidaba hingbada chatkani.” (aiōnios )
ndi kuwaphunzitsa amvere zonse zimene ndinakulamulirani. Ndipo onani, Ine ndidzakhala pamodzi ndi inu kufikira kutha kwa dziko lapansi pano.” (aiōn )
Eina nakhoida pikhiba yathang pumnamak adu ngaknaba makhoibu tambiyu. Aduga yeng-u, taibangpangi aroiba matam adu phaoba nakhoibu matam pumnamakta eina loinabigani.” (aiōn )
koma aliyense amene achitira mwano Mzimu Woyera sadzakhululukidwa pakuti wachita tchimo losatha.” (aiōn , aiōnios )
Adubu Thawai Asengbagi maiyokta thina ngangba mahakpudi keidoungeidasu kokpiroi maramdi mahakna lomba naidaba pap ama langsillabani.” (aiōn , aiōnios )
koma nkhawa zamoyo uno, chinyengo cha chuma ndi zokhumba za zinthu zina zimabwera ndi kutchinga mawu, ndipo amawachititsa kukhala osabala chipatso. (aiōn )
adubu taibangpan punsi asigi langtaknaba, lanthumgi oiba nungaibagi lounam amadi makhal kayagi apambasingna makhoida changkhiduna Mapu Ibungogi wahei adu namhatkhi aduga mahei yalhande. (aiōn )
Ngati dzanja lako likuchimwitsa, lidule. Ndi kwabwino kwa iwe kulowa mʼmoyo ndi dzanja limodzi kusiyana ndi kukhala ndi manja awiri ndi kupita ku gehena, kumene moto wake suzima. (Geenna )
Maram aduna nahakki khutna nahakpu papta tahallabadi, madu kakthatkho. Maramdi nakhut ani pallaga norokki mutnaidaba meida langsinbabudi, nakhut namata panduna hingbada changbana nahakkidamak henna phei. (Geenna )
Ndipo ngati phazi lako likuchimwitsa, lidule. Ndi kwabwino kwa iwe kulowa mʼmoyo olumala kusiyana ndi kukhala ndi mapazi awiri ndi kuponyedwa mu gehena. (Geenna )
Nahakki khongna nahakpu papta tahallabadi, madu kakthatkho. Maramdi nakhong ani pallaga norokta langsinbabudi, nakhong nama yaodana hingbada changbana nahakkidamak henna phei. (Geenna )
Ndipo ngati diso lako likuchimwitsa, likolowole. Ndi kwabwino kwa iwe kulowa ufumu wa Mulungu ndi diso limodzi, kusiyana ndi kukhala ndi maso awiri ndi kuponyedwa mu gehena, (Geenna )
Nahakki mitna nahakpu papta tahallabadi, madu kotthokkho. Maramdi namit ani pallaga norokta langsinbabudi, namit namatang pallaga Tengban Mapugi leibakta changbana nahakkidamak henna phei. (Geenna )
Yesu atanyamuka, munthu wina anamuthamangira nagwa mogwada pamaso pake. Iye anafunsa kuti, “Aphunzitsi abwino, ndichite chiyani kuti ndilandire moyo wosatha?” (aiōnios )
Adudagi Jisuna maphamdu thadoklamlaga lambida asum lakpada nupa amana chellaklaga Ibungogi mangda khuru khudak kunladuna Ibungoda hangjarak-i, “Aphaba Oja Ibungo, lomba naidaba punsi phangjanaba eina kari toujagadage?” (aiōnios )
adzalephera kulandira 100 (nyumba, abale, alongo, amayi, ana ndi minda, pamodzi ndi mazunzo) mʼbado uno ndi moyo wosatha nthawi ya mʼtsogolo. (aiōn , aiōnios )
taibangpanda leiringei matamda mayum-makei, machin-manao, machan-mache, mama, macha, amadi lou-singgi saruk chama chama henna phangjagani aduga loinana otpi neibiba amasung lakkadaba matam aduda lomba naidaba punsi phangjagani. (aiōn , aiōnios )
Ndipo Iye anati kwa mtengo, “Palibe amene adzadyenso chipatso kuchokera kwa iwe.” Ndipo ophunzira ake anamva Iye akunena izi. (aiōn )
Adudagi Jisuna heiyit pambi aduda hairak-i, “Kana amatana nangondagi mahei amuk hanna chadasanu.” Aduga Ibungona haiba adu tung-inbasing aduna tare. (aiōn )
ndipo adzalamulira pa nyumba ya Yakobo ku nthawi zonse; ufumu wake sudzatha.” (aiōn )
Aduga mahakna Jacob-ki chada-naodasinggi ningthou oina matam pumbagi oina pan-gani, amadi mahakki leibak adu lomba nairoi.” (aiōn )
Kwa Abrahamu ndi zidzukulu zake ku nthawi zonse monga ananena kwa makolo athu.” (aiōn )
Ningsingbikhi mahakna, matam pumnamakta chanbiba utpigani haibadu, Abraham amadi mahakki charon suronsingda!” (aiōn )
(Monga mmene ananenera kudzera mwa aneneri oyera), (aiōn )
Mahakna mamangngeida mahakki wa phongdokpiba asengba maichousingi mapanna washakpikhi, (aiōn )
Ndipo ziwandazo zimamupempha mobwerezabwereza kuti asazitumize ku dzenje la mdima. (Abyssos )
Adudagi lai phattabasing aduna Ibungoda makhoibu makha naidaba komda chatnanaba yathang pibidanaba hanna hanna haijarammi. (Abyssos )
Kodi iwe Kaperenawo, adzakukweza mpaka kumwamba? Ayi, adzakutsitsa mpaka ku Malo a anthu akufa. (Hadēs )
Aduga he Capernaum! Nangbu swargada thanggatpigadra? Natte, nangdi khamnung leibakta hunthagani.” (Hadēs )
Nthawi ina katswiri wa malamulo anayimirira kuti ayese Yesu. Iye anati, “Aphunzitsi, ndichite chiyani kuti ndikhale ndi moyo wosatha?” (aiōnios )
Nongma wayel yathanggi oja amana hougatlaga Jisubu chang yengladuna wahang ama hanglak-i, “Oja Ibungo, lomba naidaba punsi phangnaba eina kari toujagadage?” (aiōnios )
Koma Ine ndidzakuonetsani amene muyenera kumuopa: Wopani Iye, amene pambuyo pakupha thupi, ali ndi mphamvu yakukuponyani ku gehena. Inde, Ine ndikuwuzani, muopeni Iye. (Geenna )
Adubu nakhoina kanabu kigadabano haibadu eina nakhoida haige. Madudi hatlaba matungda norokta langsingnaba matik leiba Tengban Mapu mahakpu kiyu. Eina nakhoida hairibasini, nakhoina kigadaba adu mahak asini. (Geenna )
“Bwana anayamikira kapitawo wosakhulupirikayo popeza anachita mochenjera. Pakuti anthu a dziko lino lapansi ndi ochenjera kwambiri akamachita zinthu ndi anthu ofanana nawo kuposa anthu a kuwunika. (aiōn )
Madugi mahei oina mapu aduna pukchel sengdaba thabak asin arang touba nupa adubu asigumba heisingba thabak asigidamak thagatlammi. Maramdi taibangpan asigi machasingna makhoigi mirol asida mangalgi machasingdagi henna sing-i.” (aiōn )
Ine ndikukuwuzani inu, gwiritsani ntchito chuma cha dziko lapansi kuti mudzipezere nokha abwenzi, kuti pamene chatha mudzalandiridwe mʼmalo okhala amuyaya. (aiōnios )
Eina nakhoida hairibasini, asumna nakhoina taibangpanbagi lan thum sijinnaduna nakhoi nasagidamak marup semmu aduga langi kanapham leitraba matam aduda makhoina nakhoibu lomba naidaba yumda lousinbigani. (aiōnios )
Ali mʼgehena kuzunzika, anakweza maso ake ndipo anaona Abrahamu ali ndi Lazaro pambali pake. (Hadēs )
Amasung khamnung leibakta mahakna awaba khangduna mathakta yengkhatpa matamda thapna Abraham amasung mahakki nakanda Lazarus leiba urammi. (Hadēs )
Oweruza wina wake anamufunsa Iye kuti, “Aphunzitsi abwino, ndichite chiyani kuti ndilandire moyo wosatha?” (aiōnios )
Nongma Jihudigi luchingba amana Jisuda asumna hanglammi, “Aphaba Oja Ibungo, lomba naidaba punsi phangjanaba eina kari toujagadage?” (aiōnios )
adzalephera kulandira mowirikiza mʼmoyo uno, ndi mʼmoyo ukubwerawo, moyo wosatha.” (aiōn , aiōnios )
mahakna taibangpanda leiringei matamda madudagi saruk yamna henna phangloidaba amasung lakkadaba matam aduda lomba naidaba punsi phangloidaba mi kana amata leite.” (aiōn , aiōnios )
Yesu anayankha kuti, “Anthu a mʼbado uno amakwatira ndi kukwatiwa. (aiōn )
Maduda Jisuna makhoida khumlak-i, “Chak asidadi misingna luhong-i, aduga machasingbu luhongnaba thajei-yonjei. (aiōn )
Koma mʼmoyo umene ukubwerawo, anthu amene adzaukitsidwe kwa akufa sadzakwatira kapena kukwatiwa. (aiōn )
Adubu sibadagi hinggatpada amadi lakkadaba matam aduda leibada matik chaba nupa nupising adunadi maduda luhonglaroi. (aiōn )
kuti aliyense amene akhulupirira Iye akhale ndi moyo wosatha. (aiōnios )
madu mahakpu thajaba mi khudingna lomba naidaba punsi phangnanabani. (aiōnios )
“Pakuti Mulungu anakonda dziko lapansi, kotero anapereka Mwana wake wobadwa yekha, kuti aliyense wokhulupirira Iye asatayike koma akhale ndi moyo wosatha. (aiōnios )
Tengban Mapuna taibangpanbabu asukki matik nungsibire aduna mahakki amatta ngairaba Machanupa adu pibire, maram aduna Machanupa adubu thajaba mi khudingna mangdaduna lomba naidaba hingba phangjananabani. (aiōnios )
Aliyense wokhulupirira Mwanayo ali ndi moyo wosatha, koma iye amene samvera Mwanayo sadzawuona moyo, pakuti mkwiyo wa Mulungu umakhala pa iye.” (aiōnios )
Machanupa adubu thajaba mi aduna lomba naidaba hingba adu phangle; Machanupa adugi wa indaba mahak aduna hingba phangloi adubu Mapu Ibungogi asaoba mahakki mathakta leigani. (aiōnios )
koma aliyense amene adzamwa madzi amene Ine ndidzamupatsa sadzamvanso ludzu. Ndithudi, madzi amene ndidzamupatsa adzakhala kasupe wamadzi wotumphukira ku moyo wosatha.” (aiōn , aiōnios )
adubu eina piba ising adu thakpa mi khudingmak adudi makhoida khourangba amuk hanna leiraroi. Eina pigadaba ising aduna makhoida hingba piba iphut oiraktuna makhoida lomba naidaba hingba pibigani.” (aiōn , aiōnios )
Ngakhale tsopano amene akukolola akulandira malipiro ake, ndipo akututa mbewu ku moyo wosatha kuti wofesa ndi wokolola asangalale pamodzi. (aiōnios )
Maru hunba mahakka akhaoba mahakka punna haraominnanaba, akhaoba mahak adu khutsuman phang-i amasung lomba naidaba hingbagi mahei khomjilli. (aiōnios )
“Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti aliyense amene amamva mawu anga ndi kukhulupirira Iye amene ananditumiza Ine, ali ndi moyo wosatha ndipo sadzaweruzidwa. Iye wachoka mu imfa ndipo walowa mʼmoyo. (aiōnios )
“Eina nakhoida tasengnamak hairiba asini, eigi wa taba amadi eibu thabirakpa Ibungo mahakpu thajaba makhoi adu lomba naidaba hingba phangle. Makhoigi mathakta wayenba leiraroi; makhoidi sibadagi hingbada hannana lanthokkhre. (aiōnios )
Inu mumasanthula malemba chifukwa mumaganiza kuti mʼmalembamo muli moyo wosatha. Awa ndi malemba amene akundichitira umboni. (aiōnios )
Nakhoina Mapugi puyabu thawai yaona neinei maramdi puyaduda nakhoina lomba naidana hingba adu phanggani haina khalli. Adubu Mapugi puya adumakna eigi maramda hairi! (aiōnios )
Gwirani ntchito, osati chifukwa cha chakudya chimene chimawonongeka koma chifukwa cha chakudya chimene sichiwonongeka mpaka ku moyo wosatha, chimene Mwana wa Munthu adzakupatsani. Mulungu Atate anamusindikiza chizindikiro chomuvomereza.” (aiōnios )
Manggadaba chinjakkidamak thabak suganu adubu lomba naidaba hingba phaoba leiba chinjak adugidamak thabaksu. Masigi chinjak asidi Migi Machanupa aduna nakhoida pibigani maramdi Tengban Mapu Mapa Ibungo aduna mangonda yabibagi khudam nambire.” (aiōnios )
Pakuti chifuniro cha Atate anga ndi chakuti aliyense amene aona Mwanayo namukhulupirira akhale ndi moyo wosatha, ndipo Ine ndidzamuukitsa kwa akufa pa tsiku lomaliza.” (aiōnios )
Eigi Ipagi aningba adudi Machanupa adubu ujaba amadi Ibungo mahakpu thajaba makhoi pumnamakna lomba naidaba hingba phangbani aduga eina makhoibu aroiba numitta hinggat-hanbigani.” (aiōnios )
Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti Iye amene akhulupirira ali nawo moyo wosatha. (aiōnios )
Eina nakhoida tasengnamak hairibasini, eibu thajaba mahak aduna lomba naidaba hingba phangle. (aiōnios )
Ine ndine chakudya chamoyo chochokera kumwamba. Ngati munthu adya chakudya ichi, adzakhala ndi moyo nthawi zonse. Chakudya chimenechi ndi thupi langa, limene Ine ndidzalipereka kuti anthu pa dziko lapansi akhale ndi moyo.” (aiōn )
Swargadagi kumtharakpa ahingba tal adu eini. Kanagumbana tal asi charabadi mahak lomba naidana hinggani. Taibangpan asina hingjanaba eina pigadouriba tal adu eigi hakchangni.” (aiōn )
Aliyense amene adya thupi langa ndi kumwa magazi anga ali ndi moyo wosatha ndipo Ine ndidzamuukitsa kwa akufa pa tsiku lomaliza. (aiōnios )
Adubu eigi hakchang charaba amadi eigi ee thaklaba mi aduna lomba naidana hingba phangle aduga eina mahakpu aroiba numitta hinggat-hanbigani. (aiōnios )
Ichi ndiye chakudya chimene chinatsika kuchokera kumwamba. Makolo athu akale anadya mana ndi kufa, koma iye amene adya chakudya ichi, adzakhala ndi moyo nthawi yonse.” (aiōn )
Masini swargadagi kumtharaklaba tal adu. Nakhoigi napa napusingna manna chakhi aduga sikhi adubu tal asi chaba mahak adudi lomba naidana hinggani.” (aiōn )
Simoni Petro anamuyankha Iye kuti, “Ambuye, ife tidzapita kwa yani? Inu muli ndi mawu amoyo wosatha. (aiōnios )
Maduda Simon Peter-na khumlak-i, “Ibungo, eikhoina kanada chatlugani? Ibungoda lomba naidaba hingba pibiba waheising adu lei. (aiōnios )
Pajatu kapolo alibe malo wokhazikika mʼbanja, koma mwana ndi wa mʼbanjamo nthawi zonse. (aiōn )
Minaidi imung aduda matam pumbagi oina leite adubu machanupa adudi matam pumbagi oina lei. (aiōn )
Ine ndikukuwuzani choonadi, munthu akasunga mawu anga, sadzafa konse.” (aiōn )
Eina nakhoida tasengnamak hairibasini, kanagumbana eigi wa illabadi mahak keidoungeidasu siraroi.” (aiōn )
Pamenepo Ayuda anafuwula kuti, “Tsopano ife tadziwadi kuti Inu ndi wogwidwa ndi chiwanda! Abrahamu anafa ndiponso aneneri, koma Inu mukunena kuti, ‘Ngati munthu asunga mawu anga, sadzafa.’ (aiōn )
Maduda makhoina Ibungoda hairak-i, “Nangonda lai phattaba sungsoi soidana changle haibasi houjikti eikhoi khangle. Abraham sikhi aduga Mapu Ibungogi wa phongdokpa maichousingsu sikhi adubu nahaknadi ‘Kanagumbana eigi wa illabadi mahak keidoungeidasu siraroi’ haina hairi. (aiōn )
Palibe amene anamvapo za kutsekula maso a munthu wobadwa wosaona. (aiōn )
Pokpadagi mit tanglakpa mi amabu uhanbiba haibasi taibangpan houbadagi kana amatana tadri. (aiōn )
Ine ndimazipatsa moyo wosatha ndipo sizidzawonongeka. Palibe amene adzazikwatula mʼdzanja langa. (aiōn , aiōnios )
Eina makhoida lomba naidaba hingba pibi aduga makhoi keidoungeidasu siraroi. Kana amatana makhoibu eigi khuttagi munba ngamloi. (aiōn , aiōnios )
Aliyense amene ali ndi moyo ndi kukhulupirira Ine sadzamwalira. Kodi iwe ukukhulupirira izi?” (aiōn )
Eingonda leiba aduga eibu thajaba mi khudingna keidoungeidasu siraroi. Nahak masi thajabra?” (aiōn )
Munthu amene amakonda moyo wake adzawutaya, pamene munthu amene amadana ndi moyo wake mʼdziko lino lapansi adzawusungira ku moyo wosatha. (aiōnios )
Mahakki thawaibu nungsiba aduna madu mangjagani adubu taibangpan asida leiringeida mahakki thawaibu tukkachaba mahak aduna lomba naidana hingba phaoba madu thamgani (aiōnios )
Gulu la anthu linayankha kuti, “Ife tinamva kuchokera mʼmalamulo kuti Khristu adzakhala kwamuyaya, nanga bwanji Inu mukunena kuti, ‘Mwana wa Munthu ayenera kukwezedwa?’ Kodi Mwana wa Munthuyu ndani?” (aiōn )
Miyamsing aduna khumlak-i, “Wayel Yathangdagi eikhoina khangle adudi Christtadi matam pumnamakta hingduna leigani. Aduga ‘Migi Machanupa adu thanggatpa tai’ haina nahakna kamdouna hairibano? Migi Machanupa hairibasi kanano?” (aiōn )
Ine ndikudziwa kuti lamulo lake ndi moyo wosatha. Choncho chilichonse chimene Ine ndinena ndi chimene Atate andiwuza.” (aiōnios )
Ibungo mahakki yathangdi lomba naidana hingba aduda chingbi haiba eina khang-i. Maram aduna eina haiba khudingmak adu Ipana eingonda hainanaba haibibasingni.” (aiōnios )
Petro anati, “Ayi, Inu simudzandisambitsa konse mapazi anga.” Yesu anayankha kuti, “Ngati Ine sindisambitsa mapazi ako, ulibe gawo mwa Ine.” (aiōn )
Peter-na hairak-i, “Ibungo, Ibungona keidoungeidasu eigi khong hambiroidabani.” Maduda Jisuna khumlak-i, “Eina nahakki khong hambidrabadi nahak eihakka karisu mari leinade.” (aiōn )
Ine ndidzapempha Atate, ndipo adzakupatsani Nkhoswe ina kuti izikhala nanu nthawi zonse. (aiōn )
Eina Ipada haijagani aduga Ipana nakhoida atoppa Pangbiba ama thabirakkani aduga mahakna nakhoiga matam pumbada loinabigani. (aiōn )
Pakuti Inu munamupatsa Iye ulamuliro pa anthu onse kuti apereke moyo wosatha kwa onse amene mwamupatsa. (aiōnios )
Ibungona mangonda mi pumnamakki mathakta matik pibire madu Ibungona mangonda pibiba makhoi pumnamakta mahakna lomba naidaba hingba pinanabani. (aiōnios )
Tsono moyo wosathawo ndi uwu: Iwo akudziweni Inu, Mulungu yekhayo woona, ndi Yesu Khristu, amene Inu mwamutuma. (aiōnios )
Amatta ngairaba achumba Tengban Mapu nahakpu khangba amadi Ibungona thabirakpa Jisu Christtabu khangba asi lomba naidana hingba aduni. (aiōnios )
Chifukwa simudzasiya moyo wanga kumalo a anthu akufa, ku manda, kapena kulekerera Woyerayo kuti awole. (Hadēs )
Maramdi Ibungona eibu khamnung leibakta hundokpiroi; Nahakna nahakki Asengba Mahak adubu mongphamda pattha-pumthanhanbiroi, (Hadēs )
Davide ataoneratu zimene zinali mʼtsogolo anayankhula za kuuka kwa Khristu, kuti Iye sanasiyidwe mʼmanda, ndipo thupi lake silinawole. (Hadēs )
Tengban Mapuna tungda tourakkadaba adu David-na ukhi maram aduna mahakna Christtana sibadagi hinggatpagi maramda asumna haikhi, ‘Ibungobu khamnung leibakta hundokpide; Ibungogi hakchang mongphamda pattha-pumthahanbide.’ (Hadēs )
Iye ayenera kukhalabe kumwamba mpaka nthawi ya kukonzanso zinthu zonse monga Mulungu analonjeza kale kudzera mwa aneneri ake oyera mtima. (aiōn )
Tengban Mapugi asengba maichousinggi mapanna kuirabagi mamangda khanghanbikhibagumna, Tengban Mapuna pot pumnamakpu hanjinhanbibagi matam adu laktriba phaoba Jisudi swargada leiba tai. (aiōn )
Ndipo Paulo ndi Barnaba anawayankha molimba mtima kuti, “Ife tinayenera kuyankhula Mawu a Mulungu kwa inu poyamba. Popeza inu mwawakana ndi kudziyesa nokha osayenera moyo wosatha, ife tsopano tikupita kwa anthu a mitundu ina. (aiōnios )
Adubu Paul amadi Barnabas-na thouna phana paokhum pirak-i, “Eikhoina Tengban Mapugi wa adu nakhoida hanna haiba tabani adubu nakhoina madu loudrabanina nakhoi lomba naidana hingba phangba matik chade haina nasana khanjare. Houjikti eikhoi nakhoibu thadoktuna Jihudi nattaba phurupsingda chatlagani. (aiōnios )
Anthu a mitundu ina atamva izi, anakondwa ndipo analemekeza Mawu Ambuye; ndipo onse amene anawasankha kuti alandire moyo osatha anakhulupirira. (aiōnios )
Jihudi nattaba mising aduna madu tabada makhoi haraorammi amadi Mapu Ibungogi wa adu thagatcharammi aduga lomba naidana hingba phangnaba khandokpirabasingna thajare. (aiōnios )
zinaululidwa kuyambira kalekale.’ (aiōn )
Matam kuirabagi mamangda khanghanbiraba Mapu Ibungona masi haibire.’” (aiōn )
Pakuti kuyambira pamene dziko lapansi linalengedwa, zinthu zosaoneka za Mulungu, mphamvu zake zosatha ndi chikhalidwe cha umulungu, zakhala zikuoneka bwinobwino. Akhala akuzindikira poona zimene Mulungu analenga, kotero kuti anthu sangathe kuwiringula. (aïdios )
Maramdi taibangpan asi semba matamdagi houna uba ngamdaba Ibungo mahakki magunsing haibadi Ibungo mahakki lomba naidaba panggal amadi Tengban Mapugi oiba magun adu Tengban Mapuna sembikhrabasing adudagi mayek sengna ujei amadi khangba ngammi, maram asina makhoigi ngakpipham leite. (aïdios )
Iwo anasinthanitsa choonadi cha Mulungu ndi bodza ndipo anapembedza ndi kutumikira zinthu zolengedwa mʼmalo mwa Mlengi amene ali woyenera kutamandidwa mpaka muyaya. Ameni. (aiōn )
Makhoina Tengban Mapugi achumba adubu minambaga onthoknare aduga matam pumnamakta thagatkadaba Sembiba Mapubu khurumjabagi mahutta Tengban Mapuna sembikhraba khutsemsingda makhoina khurumduna thougal toure. Amen. (aiōn )
Iye adzapereka moyo wosatha kwa amene amafunafuna ulemerero, ulemu ndi moyo pochita ntchito zabwino mopirira. (aiōnios )
Khaangheibaga loinana aphaba touriba, matik mangal, ikai khumnaba amasung mangba naidaba hingba thiriba makhoida Tengban Mapuna lomba naidaba hingba pibigani. (aiōnios )
Choncho monga momwe tchimo linkalamulira anthu ndi kubweretsa imfa pa iwo, chomwecho kunali koyenera kuti chisomo chilamulire pobweretsa chilungamo kwa anthu, ndi kuwafikitsa ku moyo wosatha mwa Yesu Khristu Ambuye athu. (aiōnios )
masi papna sibagi mapanna panbagumna eikhoigi Mapu Ibungo Jisu Christtagi mapanna lomba naidaba hingba puraknaba thoujalnasu achumba chatpagi mapanna pannabani. (aiōnios )
Koma tsopano pakuti inu mwamasulidwa ku tchimo ndipo mwasanduka akapolo a Mulungu, phindu lomwe mulipeza ndi kuyera mtima ndipo chotsatira chake ndi moyo wosatha. (aiōnios )
Adubu houjikti nakhoi paptagi naning tamhanduna Tengban Mapugi minaising oire, madugi tongjabadi nakhoigi punsi adu mapung phana Tengban Mapuda katchare, madugi maheidi lomba naidaba hingbani. (aiōnios )
Pakuti malipiro a tchimo ndi imfa, koma mphatso yaulere imene Mulungu amapereka ndi moyo wosatha mwa Khristu Yesu Ambuye athu. (aiōnios )
Maramdi papki atoumandi sibani, adubu Tengban Mapugi khudoldi eikhoigi Ibungo Christta Jisuda lomba naidaba hingbani. (aiōnios )
Awo ndi makolo athu. Kuchokera kwa iwo mʼthupi ndi kumene kunachokera makolo a Khristu Yesu amene ndi Mulungu wolamulira zinthu zonse, alemekezeke mpaka muyaya! Ameni. (aiōn )
makhoising asi masak nairaba Hebrew ipa ipusinggi chada naodani; mioiba ama oina Christtasu makhoigi phuruptagini. Pumnamakki mathakta panbiriba Tengban Mapu mangonda lomba naidana thagatpa oisanu! Amen. (aiōn )
“kapena ‘Ndani adzatsikira ku dziko la anthu akufa?’” (ndiko, kukamutenga Khristu kwa akufa). (Abyssos )
“nattraga, Kanana makha naidaba komda kumthagani?” (Madudi Christtabu asibasinggi maraktagi pukhatpani). (Abyssos )
Pakuti Mulungu anasandutsa anthu onse a mʼndende ya kusamvera kuti Iye akaonetse chifundo kwa onse. (eleēsē )
Maramdi Tengban Mapuna mioi pumnamakta chanbiba utnaba mahakna mioi pumnamakpu haiba indabadagi phadok oihalle. (eleēsē )
Pakuti zinthu zonse nʼzochokera kwa Iye, nʼzolengedwa ndi Iye ndipo zimabweretsa ulemerero kwa Iye. Kwa Iye kukhale ulemerero mpaka muyaya! Ameni. (aiōn )
Maramdi pot pumnamak Ibungona semkhibani aduga pot pumnamak Ibungogi mapanna amadi Ibungogidamak leibani. Matik mangal matam pumnamakki oina Tengban Mapugi oirasanu! Amen. (aiōn )
Musafanizidwenso ndi makhalidwe a dziko lino koma musandulike pokonzanso maganizo anu. Ndipo mudzadziwa ndi kuzindikira chifuniro chabwino cha Mulungu chomwe ndi chokondweretsa ndi changwiro. (aiōn )
Aduga taibangpan asigi sakwong louganu, adubu nakhoigi pukning nouhanduna sakwong onthok-u. Maduna Tengban Mapugi aphaba, Ibungo mahakpu pelhanba amadi mapung phaba aningba adu nakhoina khangba ngamgani. (aiōn )
Tsopano kwa Iye amene ali ndi mphamvu yokhazikitsa monga mwa uthenga wanga wabwino ndikulalikidwa kwa Yesu Khristu, monga mwa vumbulutso lachinsinsi chobisika kwa nthawi yayitali, (aiōnios )
Eikhoina Tengban Mapuda matik mangal pirasi! Jisu Christtagi maramda eina sandokpa Aphaba Paogi matung inna amadi mamangeida matam kuina lottuna thamlaklaba athuppa achumba adubu phongdokpiba adugi matung inna, Ibungo mahakna nakhoigi thajabada nakhoibu chetna lep-hanba ngam-i. (aiōnios )
koma tsopano chavumbulutsidwa ndi kudziwika kudzera mʼMalemba a uneneri mwa lamulo la Mulungu wosatha, kuti mitundu yonse ikhulupirire ndi kumvera Iye, (aiōnios )
Adubu houjikti Tengban Mapugi wa phongdokpiba maichousingna ibirambasing adugi mapanna phongdokpire; aduga lomba naidaba Tengban Mapu mahakki yathangna phurup pumnamakta khanghanbire, maduna makhoi pumnamakna thajaraktuna haiba innanabani. (aiōnios )
kwa Mulungu yekhayo wanzeru kukhale ulemerero kwamuyaya kudzera mwa Yesu Khristu! Ameni. (aiōn )
Amatta ngaiba ikhang khangba Tengban Mapuda Jisu Christtagi mapanna matam pumnamakta thagatpa oisanu. Amen. (aiōn )
Munthu wanzeru ali kuti? Munthu wozama ndi maphunziro ali kuti? Munthu wodziwa zakuya zamakono ali kuti? Kodi Mulungu sanazipusitse nzeru za dziko lapansi? (aiōn )
Adu oirabadi, asingba mi kadaida leibage? Wayel yathanggi oja kadaida leibage? Taibangpan asigi yetnaba heiba akhang aheising kadaida leibage? Tengban Mapuna taibanpan asigi lousing adu apangbani haina utpikhraba nattra? (aiōn )
Komabe ife timayankhula uthenga wa nzeru kwa okhwima, koma osati ndi nzeru ya mʼbado uno kapena ya olamula a mʼbado uno, amene mphamvu yawo ikutha. (aiōn )
Adumakpu thawaida mapungpharaba makhoising aduda eina lousinggi wa ngangngi. Adubu madu taibangpan asigi lousing natte aduga aremba oiragadaba, taibangpan asida pallibasing adugi lousingsu natte. (aiōn )
Ayi, ife timayankhula za nzeru yobisika ya Mulungu, nzeru imene inabisidwa ndipo imene Mulungu anatikonzera mu ulemerero wathu isanayambe nthawi. (aiōn )
Adubu eikhoina ngangthokliba lousing asidi Tengban Mapuna mioibasingdagi lottuna thambiramba adubu taibangpan leisemdringei mamangdagi eikhoigi matik mangalgidamak hanna langduna thambiramlaba Tengban Mapugi athuppa lousing aduni. (aiōn )
Palibe olamulira aliyense wa mʼbado uno amene anamumvetsetsa popeza anakamumvetsetsa sakanamupachika Ambuye wa ulemerero. (aiōn )
Taibangpan asigi leingakpa kananasu lousing asibu khangkhide. Karigumba makhoina masibu khanglamlabadi makhoina matik mangalgi Ibungobu cross-ta hatlamloidabani. (aiōn )
Choncho musadzinyenge. Ngati wina wa inu akuganiza kuti ndi wanzeru pa mulingo wa mʼbado uno, ayenera kukhala “wopusa” kuti athe kukhala wanzeru. (aiōn )
Mi kana amatana masana masabu minamdasanu. Aduga nakhoigi naraktagi kanagumbana taibangpan asigi machat matung-inna masa mathantabu asingbani khanjarabadi mahakna tasengna asingba oiraknaba mahakna apangba oiraksanu. (aiōn )
Nʼchifukwa chake ngati zimene ine ndimadya zichititsa mʼbale wanga kugwa mu tchimo, sindidzadyanso chakudyacho kuti mʼbaleyo ndisamuchimwitse. (aiōn )
Maram aduna eina chariba pot aduna eigi ichil inaobu papta tahallabadi, eina mahakpu papta tahandanaba ei keidounungdasu sa sukcha chararoi. (aiōn )
Zinthu izi zinawachitikira kuti zikhale chitsanzo ndipo zinalembedwa kuti zikhale chenjezo kwa ife, amene tiyandikira nthawi ya kutha kwa zonse. (aiōn )
Masi pumnamaksing asi atoppasingda pandam oinaba makhoida thokkhibani aduga makhoina aroiba matam asida hingliba eikhoida cheksin-wa oinaba irambani. (aiōn )
“Iwe imfa, kupambana kwako kuli kuti? Iwe imfa, ululu wako uli kuti?” (Hadēs )
“Siba, nahakki lanngamba adu kadaidano? Siba, nahakki mamu adu kadaida leibage?” (Hadēs )
Mulungu wa dziko lapansi anachititsa khungu anthu osakhulupirira, kuti asathe kuona kuwala kwa Uthenga Wabwino umene umaonetsa ulemerero wa Khristu, amene ndi chifaniziro cha Mulungu. (aiōn )
Makhoina thajade maramdi Tengban Mapugi sak-ong oiriba Christtagi matik mangalgi Aphaba Pao adubu makhoina uba ngamdananaba makhoigi pukningbu taibangpanba asigi phattaba lai aduna mamit tanghalle. (aiōn )
Pakuti masautso athu ndi opepuka ndi a kanthawi, koma akutitengera ulemerero wamuyaya umene ndi wopambana kwambiri. (aiōnios )
Maramdi ngaihakki oiba karisu nattaba eikhoigi awa anangsing asina makhoidagi yamna henba lomba naidaba matik mangal adu eikhoida pubirakkani. (aiōnios )
Motero sitiyangʼana zinthu zimene ndi zooneka ndi maso, koma zinthu zimene ndi zosaoneka. Pakuti zimene zimaoneka ndi zosakhalitsa, koma zimene sizioneka ndi zamuyaya. (aiōnios )
Maram aduna eikhoina uba ngamba potsing aduda yengdaduna uba ngamdaba aduda mityeng chetna thamjei. Maramdi eikhoina uribasing asidi matam kharakhaktanggini adubu uba ngamdaba adudi lomba naidabagini. (aiōnios )
Popeza tikudziwa kuti ngati msasa wa dziko lapansi umene tikukhalamo uwonongeka, tili ndi nyumba yochokera kwa Mulungu, nyumba yamuyaya yakumwamba, osati yomangidwa ndi manja a anthu. (aiōnios )
Maramdi eikhoina leiriba phiyum haibadi eikhoigi taibang hakchang asina mangkhrabada mioibagi khutna saba nattaba, Tengban Mapugi oiba, lomba naidana leigadaba yum eikhoigi lei haiba eikhoina khang-i. (aiōnios )
Paja analemba kuti, “Wopereka mphatso zake mowolowamanja kwa osauka, chilungamo chake chimanka mpaka muyaya.” (aiōn )
Masi Mapugi Puyada ikhibagumbani, “Awatpa leibasingda mahakna marang kaina pinabi; Mahakki chanbi-heiba adu matam pumnamakta lengdana lei.” (aiōn )
Mulungu, Atate a Ambuye Yesu, amene tiyenera kumutamanda nthawi zonse, akudziwa kuti sindikunama. (aiōn )
Ibungo Jisugi Tengban Mapusu, Mapasu oiriba lomba naidana thagatchagadaba Ibungo mahakna eina minamba ngangde haibasi khangbi. (aiōn )
Yesuyo anadzipereka yekha chifukwa cha machimo athu kuti atipulumutse ku njira za moyo woyipa uno, molingana ndi chifuniro cha Mulungu ndi Atate athu. (aiōn )
Eikhoibu houjikki phattraba chak asidagi kanbinaba eikhoigi Tengban Mapu amadi Ipa adugi aningba adubu injaduna eikhoigi papkidamak Christtana masamakpu katthokpire. (aiōn )
Ulemerero ukhale kwa Mulunguyo mpaka muyaya. Ameni. (aiōn )
Lomba naida naidana Tengban Mapuda matik mangal oisanu. Amen! (aiōn )
Pakuti amene amafesa zokondweretsa thupi lake la uchimo, kuchokera ku khalidwe limenelo adzakolola chiwonongeko; amene amafesa zokondweretsa Mzimu, kuchokera kwa Mzimu adzakolola moyo wosatha. (aiōnios )
Maramdi masagi hakchangbu pelhannaba hunba mahak aduna hachangdagi amangba lokchagani; adubu Thawai adubu pelhannaba hunba mahak aduna Thawai adudagi lomba naidana hingba lokchagani. (aiōnios )
Anamukhazika pamwamba pa ulamuliro onse ndi mafumu, mphamvu ndi ufumu, ndiponso pamwamba pa dzina lililonse limene angalitchule, osati nthawi ino yokha komanso imene ikubwerayo. (aiōn )
Christtana swargagi leingakpasing, matiksing, pangalsing amasung mapusing pumnamakki mathakta palle; amadi taibangpan asidata nattana lakkadaba adudasu Christtagi mingna matik pumnamakki minggi mathakta lei. (aiōn )
mmene inu munkakhalamo pamene munkatsatira njira za dziko lapansi ndi za ulamuliro waufumu wa mlengalenga, mzimu umene ukugwira ntchito tsopano mwa amene samvera. (aiōn )
Matam aduda nakhoina taibangpangi oiba phattaba machat adugi matung illammi; malangda leiriba thawaigi panggalsinggi mapu adugi, haibadi Tengban Mapuna haiba indaba mising adubu houjik makhada thamliba thawai aduna haiba induna leirammi. (aiōn )
ndi cholinga chakuti mʼnthawi imene ikubwera, Iyeyo adzaonetse chuma choposa cha chisomo chake, choonetsedwa mwa kukoma mtima kwake kwa ife mwa Khristu Yesu. (aiōn )
Masi mahakna Christta Jisuda, eikhoida utpikhiba nungsiba aduda phongdokpiriba changdamningai leitana marang kairaba mahakki thoujal adu lakkadaba matam pumnamakta utpinanabani. (aiōn )
Ndinasankhidwa kuti ndifotokoze momveka bwino kwa munthu aliyense za chinsinsi chimenechi, chinsinsi chimene kuyambira kale chinali chobisika mwa Mulungu amene analenga zinthu zonse. (aiōn )
Amasung Tengban Mapugi athuppa thourang adu kamdouna mahei yalhan-gadage haibadu mipum khudingmakta uhannaba khudongchaba adu iphamda pinabire. Athupa asi pot pumnamakpu sembiba Mapu, Tengban Mapuna houkhraba miron pumnamakta thuptuna thamlammi. (aiōn )
Chimenechi chinali chikonzero chamuyaya cha Mulungu, chimene chinachitika kudzera mwa Khristu Yesu Ambuye athu. (aiōn )
Tengban Mapuna masi eikhoigi Ibungo Christta Jisugi mapanna thunghanbikhraba mahakki lomba naidraba thourang adugi matung inna toubani. (aiōn )
Iyeyo akhale ndi ulemu mu mpingo ndi mwa Khristu Yesu pa mibado yonse mpaka muyaya. Ameni. (aiōn )
Singlupta amadi Christta Jisuda, matam pumnamakta lomba naida naidana Tengban Mapugi matik mangal oirasanu! Amen. (aiōn )
Pakuti sitikulimbana ndi thupi ndi magazi, koma tikulimbana ndi maufumu, maulamuliro, mphamvu za dziko la mdima, ndi mphamvu zoyipa kwambiri zauzimu zamlengalenga. (aiōn )
Maramdi eikhoina mioibagi maiyokta lanthengnaba natte adubu swargagi maphamsingda leiriba phattaba thawaisinggi oiba panggalsing, leingakpasing, matiksing, amadi amamba taibanpan asigi panggalsing aduga lanthengnabani. (aiōn )
Kwa Mulungu ndi Atate athu, kukhale ulemerero mpaka muyaya. Ameni. (aiōn )
Eikhoigi Tengban Mapu amasung Ipa Ibungoda lomba naidana matik mangal oisanu. Amen. (aiōn )
chinsinsi chimene chakhala chikubisika kwa nthawi ndi mibado, koma tsopano chawululidwa kwa oyera mtima. (aiōn )
athuppa adu houkhraba chahi kaya kaya amadi mirol kaya kaya lottuna thamlakpani adubu houjikti Mapu Ibungogi misinggi maphamda phongdokpire. (aiōn )
Adzalangidwa ndi chiwonongeko chamuyaya ndipo sadzaonanso nkhope ya Ambuye ndi ulemerero wamphamvu zake (aiōnios )
Makhoi adu Ibungogi mangdagi amasung Ibungogi matik mangal panggalgi adudagi khaidoktuna lomba naidaba amang-atagi cheirak khaanggani. (aiōnios )
Ambuye athu Yesu Khristu mwini ndi Mulungu Atate wathu, amene anatikonda ife ndipo mwachisomo chake anatipatsa kulimba mtima kwamuyaya ndi chiyembekezo chabwino, (aiōnios )
Houjik, eikhoigi Ibungo Jisu Christta masamakna amasung eikhoibu nungsibiba eikhoigi Ipa Ibungo Tengban Mapu amadi mahakki thoujalna eikhoida lomba naidana thougatpiba amadi aphaba asha pinabisanu. (aiōnios )
Ndipo pa chifukwa chimenechi, Mulungu anandichitira chifundo, kuti mwa ine, wochimwitsitsa, Khristu Yesu aonetse kuleza mtima kwake konse kuti ndikhale chitsanzo cha omwe angathe kumukhulupirira ndi kulandira moyo wosatha. (aiōnios )
Adum oinamak maram asigidamak haibadi pap chenbasinggi marakta khwaidagi pap chenba eingonda Tengban Mapuna chanbiba adu utpire, madu Ibungo mahakpu tungda thajagababa amadi lomba naidaba punsi phanggadaba mi pumnamakta Christta Jisuna mahakki kuina khaangheiba adu pandam oina utpinanabani. (aiōnios )
Tsopano kwa Mfumu yamuyaya, yosafa, yosaoneka, amene Iye yekha ndiye Mulungu, kukhale ulemu ndi ulemerero mpaka muyaya. Ameni. (aiōn )
Lomba naidaba Ningthou, siba naidraba, uba ngamdaba, amatta ngairaba Tengban Mapu Ibungo mangonda matam pumnamakta ikai khumnaba amasung matik mangal leiba oirasanu! Amen. (aiōn )
Menya nkhondo yabwino yachikhulupiriro. Gwiritsitsa moyo wosatha umene anakuyitanira pamene unavomereza bwino lomwe pamaso pa mboni zambiri. (aiōnios )
Thajabagi akanba laan adu soknou. Lomba naidaba hingba adu chetna paiyu masida nahakpu koubire amasung sakhi kayagi mamangda nahakna phongdokle. (aiōnios )
Ndiye yekha wosafa ndipo amakhala mʼkuwala koopsa. Mulungu amene munthu aliyense sanamuone. Kwa Iye kukhale ulemu ndi mphamvu mpaka muyaya. Ameni. (aiōnios )
Sinaidaba asi Ibungo Mahak khaktani amadi kananasu changsinba ngamdaba mangal aduda Ibungo mahak lei. Aduga kana amatana Ibungo mahakpu ukhidri amasung ubasu ngamde. Ibungo mangonda ikai khumnaba amasung lomba naidana panggal leiba oirasanu! Amen. (aiōnios )
Anthu onse amene ali ndi chuma uwalamule kuti asanyade kapena kuyika mitima yawo pa chuma chimene nʼchosadalirika. Koma chiyembekezo chawo chikhale mwa Mulungu amene amatipatsa mowolowamanja zonse zotisangalatsa. (aiōn )
Houjikki taibangpanba asida inakkhullibasing makhoina pukning nawangdanaba amadi areppa leitaba landa asa thamdanaba adubu eikhoibu nungainanaba pot pumnamak marang kaina pibiba Tengban Mapuda makhoigi asa thamjanaba yangthang piyu. (aiōn )
Iye anatipulumutsa ndipo anatiyitanira ku moyo oyera mtima, osati chifukwa cha chilichonse chimene tinachita, koma chifukwa cha chikonzero ndi chisomo chake. Chisomo chimenechi anatipatsa ife mwa Khristu Yesu nthawi isanayambe. (aiōnios )
Ibungona eikhoibu kanbire amasung Ibungo mahakmakki mi oinaba eikhoibu koubire, masi eikhoina toukhiba karigumba thabak amagidamak natte adubu Ibungo mahakki ningba amasung thoujalgi matung innani. Thoujal asi taibang leisemdringei mamangda Christta Jisugi mapanna eikhoida pibire, (aiōnios )
Choncho ndikupirira chilichonse chifukwa cha osankhidwa, kuti nawonso apulumutsidwe ndi Khristu Yesu ndi kulandira ulemerero wosatha. (aiōnios )
Maram aduna lomba naidaba matik mangalga loinana Christta Jisuda leiba aran-khubham adu Tengban Mapuna khandoklaba makhoinasu phangnanaba eina makhoigidamak pumnamak khaang-i. (aiōnios )
Paja Dema anandisiya chifukwa chokonda dziko lapansi lino, ndipo anapita ku Tesalonika. Kresike anapita ku Galatiya ndipo Tito anapita ku Dalimatiya. (aiōn )
maramdi Demas-na houjikki taibangpan asibu nungsibadagi eibu thadoklamlaga Thessalonica-da chatkhre. Crescens-su Galatia-da, aduga Titus-na Dalmatia-da chatkhre. (aiōn )
Ambuye adzandilanditsa ku chilichonse chofuna kundichita choyipa ndipo adzandisamalira bwino mpaka kundilowetsa chonse mu ufumu wake wakumwamba. Kwa Iye kukhale ulemerero mpaka muyaya. (aiōn )
Eingonda phattaba landarakpa pumnamaktagi Mapu Ibungona kanbigani aduga Ibungo mahakki swarga Leibakta eibu asoi angam yaodana pubigani. Ibungoda matam pumnamakta matik mangal leiba oirasanu! Amen. (aiōn )
ndi kuwapatsa chiyembekezo cha moyo wosatha, umene Mulungu amene sanama, analonjeza nthawi isanayambe. (aiōnios )
Minamba ngangdaba Tengban Mapuna leisemdringei mamangdagi eikhoida hingba asigidamak wasakpibani, (aiōnios )
Chisomo chimatiphunzitsa kukana moyo osalemekeza Mulungu komanso zilakolako za dziko lapansi. Ndipo chimatiphunzitsa kukhala moyo odziletsa, olungama ndi opembedza Mulungu nthawi ino, (aiōn )
Tengban Mapu ningdaba amasung taibangpan-gi oiba apamba adu thadoktuna, isa khudum chanjaba, pukchel tingba, amadi ngasigi taibangpan asida laining chetpa punsi ama hingnaba thoujal asina eikhoibu tambi, (aiōn )
kuti titalungamitsidwa mwachisomo chake, tikhale olowamʼmalo okhala ndi chiyembekezo cha moyo wosatha. (aiōnios )
masi Ibungo mahakki thoujalna eikhoibu chumhanbinabani aduga eikhoina asa toujaba lomba naidaba hingba adu phangnanabani. (aiōnios )
Mwina chifukwa chimene unasiyana naye kwa kanthawi ndi chakuti ukhale nayenso nthawi zonse. (aiōnios )
Matam khara mahak nangondagi khainaramba asi nahakna mahakpu matam pumbagi oina phangjaba yananaba oiramba yai. (aiōnios )
Koma masiku otsiriza ano, Mulungu wayankhula nafe kudzera mwa Mwana wake. Mwanayu anamusankha kuti akhale mwini wa zinthu zonse, ndiponso Mulungu analenga dziko lonse kudzera mwa Iye. (aiōn )
adubu aroiba numitsing asidadi Ibungo mahakna mahakki Machanupagi mapanna eikhoida wa ngangbire. Ibungo mahakki mapanna Tengban Mapuna taibangpan pumba sembi aduga aroibada Tengban Mapuna Ibungo mahakpu pot pumnamakki mapu oinanaba khandokpire. (aiōn )
Koma za Mwana wake akuti, “Inu Mulungu, mpando wanu waufumu udzakhala mpaka muyaya, ndipo mudzaweruza molungama mu ufumu wanu. (aiōn )
Adubu Machanupa adugi maramda Tengban Mapuna hairak-i, “He Tengban Mapu, nahakki leibakti loiba naidana matam pumnamakki oina leigani! Nahakna nahakki misinggi mathakta achumba wayen-ga loinana pan-gani. (aiōn )
Ndipo penanso anati, “Iwe ndiwe wansembe mpaka muyaya, monga mwa unsembe wa Melikizedeki.” (aiōn )
Asengba puyagi atoppa mapham amadasu Tengban Mapuna asumna haikhi, “Melchizedek-ki matougumna nahakti lomba naidana purohitni.” (aiōn )
Atasanduka wangwiro kotheratu, anakhala gwero la chipulumutso chosatha kwa onse omvera Iye. (aiōnios )
Mahakpu mapung phahallabada, mahakna haiba inba makhoi pumnamakkidamak mahak asi lomba naidaba aran-khubham phangjapham oirakkhi. (aiōnios )
za maubatizo, za kusanjika manja, za kuuka kwa akufa ndi za chiweruzo chotsiriza. (aiōnios )
baptize toubagi, amadi khut thambagi maramda tambiba; sibadagi hinggatpa amadi lomba naidaba wayenba hairiba hiramsing asigi yumpham amuk hanjinna tholloidabani. (aiōnios )
Analawa kukoma kwa mawu a Mulungu ndi mphamvu za nthawi ikubwera. (aiōn )
Tengban Mapugi waheidi aphabani haiba amadi lakkadaba matam adugi panggalsing adu makhoina mahao tangkhre. (aiōn )
Yesu anatitsogolera kupita kumeneko, nalowako mʼmalo mwathu. Iye anasanduka Mkulu wa ansembe onse wamuyaya, monga mwa dongosolo la unsembe wa Melikizedeki. (aiōn )
Mapham aduda Jisuna Melchizedek-ki matougumna lomba naidaba purohitlen oiduna eikhoigidamak eikhoidagi mang thana changle. (aiōn )
Pakuti Mulungu anamuchitira umboni kuti, “Iwe ndi wansembe wamuyaya, monga mwa dongosolo la unsembe wa Melikizedeki.” (aiōn )
Maramdi Mapugi puyana hai, “Nahakti Melchizedek-ki matougumna matam pumbagi oina purohit ama oigani.” (aiōn )
Koma Yesu ankakhala wansembe ndi lumbiro pamene Mulungu anati, “Ambuye analumbira ndipo sangasinthe maganizo ake, ‘Iwe ndi wansembe wamuyaya.’” (aiōn )
Adubu Jisuna purohit oiba matamda wasakpa yao-i masi Tengban Mapuna Ibungoda haikhi, “MAPU IBUNGO-na achetpa wasak ama leple aduga madu amuk handokloi: ‘Nahak matam pumbagi oina purohit oigani.’” (aiōn )
Koma Yesu popeza ndi wamuyaya, unsembe wake ndi wosatha. (aiōn )
Adubu Jisudi lomba naidana hingba maramna mahakki purohitki thabak adu atoppa kanagumba amada sinnaba toude. (aiōn )
Pakuti lamulo limasankha anthu amene ndi ofowoka kukhala akulu a ansembe; koma lumbiro, lomwe linabwera pambuyo pa lamulo, linasankha Mwana, amene anapangidwa kukhala wangwiro kwamuyaya. (aiōn )
Moses-ki Wayel Yathangna asonba leiraba misingbu purohitlen oina khalli. Adubu Wayel Yathanggi matungda lakpa Tengban Mapuna wasakpiba amaga yaoba wasakpiba adunadi matam pumbagi oina mapung phahallaba Machanupabu purohitlen oina khanbi. (aiōn )
Iye sanalowemo ndi magazi ambuzi yayimuna, ana angʼombe amphongo, koma analowa Malo Opatulika kamodzi kokha ndi magazi ake, atatikonzera chipulumutso chosatha. (aiōnios )
Hameng amadi sallabagi ee-gi mapanna Ibungona changkhide; adubu Ibungona Khwaidagi Asengba Mapham aduda amuktanggi oina mahak masamakki ee-gi mapanna changle aduga eikhoigidamak lomba naidaba aran-khubham pubirakle. (aiōnios )
nʼkoposa kotani magazi a Khristu, amene mwa Mzimu wamuyaya anadzipereka yekha kwa Mulungu kukhala nsembe yopanda chilema. Iye adzayeretsa chikumbumtima chathu pochotsa ntchito za imfa, kuti ife titumikire Mulungu wamoyo. (aiōnios )
Masina achumba oibanina Christtagi ee-nadi kayagi matik amukka henna thabak pangthokkani! Lomba naidaba Thawaigi mapanna Ibungona masamakpu mapungphaba iratpot oina Tengban Mapuda katpire. Eikhoina ahingba Tengban Mapubu thougal touba yananaba Ibungogi ee-na eikhoigi achum aran khangba pukningbu kanadaba laininggi oiba chatnabisingdagi sengdokpigani. (aiōnios )
Pa chifukwa chimenechi Khristu ndi mʼkhalapakati wa pangano latsopano, kuti iwo amene anayitanidwa alandire chuma chamuyaya, pakuti Iye tsopano anafa ngati dipo lomasula iwo ku machimo amene anachita ali pansi pa pangano loyamba lija. (aiōnios )
Tengban Mapuna koubikhraba makhoina Tengban Mapuna wasakpikhiba lomnaidaba yaipha thoujalsing adu phangnabagidamak Christtana anouba walepnabagi sillangbiba adu oibire. Masi touba yabagi maramdi ahanba walepnabagi makhada leiringei matamda misingna toukhiba aranbasing adudagi ningtamhanbinaba sibikhiba ama leikhiba adunani. (aiōnios )
Zikanatero bwenzi Khristu atamva zowawa kambirimbiri chilengedwere cha dziko lapansi. Koma tsopano anaoneka kamodzi kokha chifukwa cha onse pa nthawi yotsiriza kuti achotse tchimo podzipereka yekha nsembe. (aiōn )
Madu oirabadi mahakna taibangpan semngeidagi kayarak hanna awa khaanglamgadabani. Adubu houjikti aroiba matam naksillaklaba asida masamakpu iratpagi mapanna pap louthoknaba matam pumnamakki oina amuktang masamak phongdokpire. (aiōn )
Ndi chikhulupiriro timazindikira kuti dziko lapansi ndi la mmwamba zinapangidwa ndi Mawu a Mulungu, ndikuti zinthu zoonekazi zinachokera ku zinthu zosaoneka. (aiōn )
Tengban Mapugi waheigi mapanna taibangpan apumba sembikhi haibasi thajabagi mapanna eikhoina khang-i, maram aduna uriba pot adu uba ngamdaba pottagi sembani. (aiōn )
Yesu Khristu ndi yemweyo dzulo, lero ndi kunthawi zonse. (aiōn )
Jisu Christtadi ngarangsu ngasisu, amadi matam pumnamakta hongba leite. (aiōn )
Mulungu wamtendere, amene kudzera mʼmagazi a pangano lamuyaya anaukitsa Ambuye athu Yesu kwa akufa, amene ndi Mʼbusa wamkulu, (aiōnios )
Houjikti ingthabagi Tengban Mapu, haibadi lomba naidaba walepnabagi ee adugi mapanna yaosinggidamak athoiba Yaosenba oiriba, eikhoigi Mapu Ibungo Jisubu asibadagi hinggat-hanbiba, (aiōnios )
akupatseni chilichonse chabwino kuti muchite chifuniro chake ndipo Mulungu achite mwa ife, chimene chingamukomere kudzera mwa Yesu Khristu. Kwa Iye kukhale ulemerero ku nthawi zanthawi, Ameni. (aiōn )
mahakna mahakki aningba touhannaba nakhoida aphaba pumnamakna sem sabinaba amasung Jisu Christtagi mapanna Ibungo mahakki apenba oiba adu eikhoida toubisanu. Christtada matam pumnamakki oina matik mangal leiba oisanu! Amen. (aiōn )
Lilime nalonso ndi moto, dziko la zoyipa pakati pa ziwalo za thupi. Limawononga munthu yense wathunthu. Limayika zonse za moyo wake pa moto, ndipo moto wake ndi wochokera ku gehena. (Geenna )
Leidi meigumbani, ayol arangi taibangpanbani; leina eikhoigi hakchang kayatsinggi marakta kayat ama oiduna hakchang apumbada phattaba sandok-i, amasung mahakki punsigi khongchat pumnamak norok-maktagi lakpa meina chak-halli. (Geenna )
Popeza mwabadwanso, osati ndi mbewu imene imawonongeka, koma imene siwonongeka, ndiye kuti ndi Mawu a Mulungu amoyo ndi okhalitsa. (aiōn )
Maramdi mangba yaba marudagi nattaduna mangba yadaba marudagi hingba amasung matam pumbada lengdana leiba Tengban Mapugi waheigi mapanna nakhoibu amuk hanna pokpire. (aiōn )
koma mawu a Ambuye adzakhala mpaka muyaya.” Ndipo awa ndi mawu amene tinalalikira kwa inu. (aiōn )
adubu Mapu Ibungogi waheidi matam pumnamakta lengdana lei.” Nakhoida sandokpa Aphaba Pao adu wahei asini. (aiōn )
Ngati wina ayankhula, ayankhuledi mawu enieni a Mulungu. Ngati wina atumikira, atumikire ndi mphamvu imene Mulungu amapereka, kuti pa zonse Mulungu alemekezedwe mwa Yesu Khristu. Kwa Iye kukhale ulemerero ndi mphamvu mpaka muyaya, Ameni. (aiōn )
Kanagumba amana wa nganglabadi, makhoina Tengban Mapugi wa ngangba amagumna nganggadabani; kanagumba amana thougal tourabadi, Tengban Mapuna pibiba panggalga loinana makhoina thougal tougadabani, masina Tengban Mapubu maram khudingmakta Jisu Christtagi mapanna thagatnabani. Matik mangal amasung panggal lomba naidana Ibungo mahakkini. Amen. (aiōn )
Ndipo Mulungu wachisomo chonse, amene anakuyitanani ku ulemerero wake wamuyaya mwa Khristu, mutamva zowawa pa kanthawi, adzakukonzaninso ndi kukulimbitsani pa maziko olimba. (aiōnios )
Adubu nakhoina matam khara awaba khaanglaba matungda thoujal pumnamakki Tengban Mapuna mahakki lomba naidaba matik mangalda Christta Jisugi mapanna eikhoibu koubiraba Ibungo mahakna, nakhoibu mapung phahanbigani amasung achetpa, panggal amadi lengdraba yumpham nakhoida pibigani. (aiōnios )
Kwa Iye kukhale mphamvu mpaka muyaya, Ameni. (aiōn )
Matam pumbagi oina panggal adu Ibungo mangonda leiba oisanu! Amen. (aiōn )
Mudzalandiridwa bwino kwambiri mu ufumu wosatha wa Ambuye ndi Mpulumutsi wathu Yesu Khristu. (aiōnios )
Asumna oirabadi eikhoigi Mapu Ibungo amasung Kanbiba Mapu Jisu Christtagi lomba naidaba leibak aduda nakhoibu taramna okpigani. (aiōnios )
Pakuti Mulungu sanalekerere angelo atachimwa paja, koma anawaponya mʼndende, nawayika mʼmaenje amdima, kuwasunga kuti adzaweruzidwe. (Tartaroō )
Maramdi Tengban Mapuna pap touba swarga dutsingbu kanbidaduna norokta langthakhi, amasung mapham aduda wayennabagidamak amambada yot-hingna punduna thamle. (Tartaroō )
Koma kulani mu chisomo ndi mʼchidziwitso cha Ambuye ndi Mpulumutsi wathu Yesu Khristu. Kwa Iye kukhale ulemerero tsopano mpaka muyaya. Ameni. (aiōn )
Adubu thoujalda amadi eikhoigi Mapu Ibungo amasung Kanbiba Mapu Jisu Christtabu khangbada mathang mathang chaokhatpa oiyu. Houjik amasung lomba naidana Ibungoda matik mangal leiba oisanu! Amen. (aiōn )
Moyowo unaoneka, tinawuona ndipo tikuchitira umboni. Tikukulalikirani za moyo wosatha umene unali ndi Atate ndipo unaonekera kwa ife. (aiōnios )
Hingba adu uhanbire; eikhoina madu ujare amadi madugi maramda eikhoina sakhi pi amasung eikhoida uhanbiba amadi Mapa Ibungoga leiminnaramba lomba naidaba hingba adu eikhoina nakhoida laothok-i. (aiōnios )
Dziko lapansi likupita pamodzi ndi zilakolako zake, koma amene amachita chifuniro cha Mulungu amakhalapo mpaka muyaya. (aiōn )
Taibangpan amasung masigi apamba adu mangsillakli; adubu Tengban Mapugi aningba touba mahak adudi matam pumnamakta hingduna lei. (aiōn )
Ndipo chimene anatilonjeza nʼchimenechi: moyo wosatha. (aiōnios )
Christtana eikhoida pibigani wasakpikhiba adu asini madudi lomba naidaba hingba aduni. (aiōnios )
Aliyense amene amadana ndi mʼbale wake ndi wakupha, ndipo inu mukudziwa kuti wopha anthu mwa iye mulibe moyo wosatha. (aiōnios )
Machin manaobu tukkachaba mahak adu mihatpani, mihatpa mi amatada lomba naidaba hingba leite haiba nakhoina khang-i. (aiōnios )
Ndipo umboniwo ndi uwu: Mulungu anatipatsa moyo wosatha, ndipo moyowu uli mwa Mwana wake. (aiōnios )
Sakhi adu asini, Tengban Mapuna eikhoida lomba naidaba hingba pibire, aduga hingba adu mahakki Machanupa aduda lei. (aiōnios )
Ine ndikulemba zimenezi kwa inu, amene mwakhulupirira dzina la Mwana wa Mulungu kuti mudziwe kuti muli ndi moyo wosatha. (aiōnios )
Tengban Mapugi Machanupagi mingda thajaba nakhoida lomba naidaba hingba lei haibasi nakhoina khangnanaba waramsing asi eina nakhoida i-bani. (aiōnios )
Tikudziwa kuti Mwana wa Mulungu anafika ndipo anatipatsa nzeru, kuti timudziwe Iye amene ali woona. Ndipo ife tili mwa Iye amene ndi woona, Mwana wake, Yesu Khristu. Iye ndi Mulungu woona ndi moyo wosatha. (aiōnios )
Eikhoina achumba Tengban Mapu adubu khangnanaba Tengban Mapugi Machanupa adu lengbiraktuna eikhoida wakhal taba pibire haibasu eikhoina khang-i. Tengban Mapugi Machanupa Jisu Christtada leijaduna eikhoina Tengban Mapuda lei. (aiōnios )
Timakukondani chifukwa cha choonadi chimene chimakhala mwa ife ndipo chidzakhala mwa ife mpaka muyaya. (aiōn )
eikhoida leiba amasung eikhoiga matam pumnamakta leiminnagadaba achumba adugi maramdani. (aiōn )
Ndipo mukumbukire angelo amene sanakhutire ndi maudindo awo, koma anasiya malo awo. Angelo amenewa Mulungu anawamanga ndi maunyolo osatha, ndipo akuwasunga mʼmalo a mdima mpaka tsiku lalikulu lachiweruzo. (aïdios )
Aduga masagi angambagi pham adu ngaktaduna makhoina leigadaba mapham adu thadokkhiba swarga dutsing adubu Ibungo mahakna achouba Numit aduda wayennabagidamak makhoibu lomba naidaba yot-hling phalangna punduna amambada thamle. (aïdios )
Musayiwale mizinda ya Sodomu ndi Gomora ija, ndi mizinda yoyandikana nayo. Anthu mʼmenemo anadziperekanso kuchita zadama ndi kuchita zonyansa zachilendo. Mizinda imeneyi yakhala ngati chitsanzo cha amene adzalangidwa ndi moto wosatha. (aiōnios )
Masiga manana Sodom amasung Gomorrah, aduga madugi akoibada leiba saharsing adugi misingnasu nupa nupigi oiba lamchat kamba sajatsingda makhoi masasing pithoklammi. Makhoibu lomba naidaba meigi cheirak pigadabasing adugi pandam oina thamle. (aiōnios )
Iwowa ali ngati mafunde awukali apanyanja, amene amatulutsa thovu la zonyansa zawo. Amenewa ali ngati nyenyezi zosochera, ndipo Mulungu akuwasungira mdima wandiweyani mpaka muyaya. (aiōn )
Makhoidi masagi ikaibabu konggolgum kahalliba ipakki akanba ithaksingni; koipai paiba thawanmichaksingni, makhoigidamak khwaidagi mamba mapham ama khaaktuna thamle. (aiōn )
Khalani mʼchikondi cha Mulungu pamene mukudikira chifundo cha Ambuye athu Yesu Khristu kuti akubweretsereni moyo wosatha. (aiōnios )
nakhoibu lomba naidaba hingbada chingbinaba eikhoigi Mapu Ibungo Jisu Christtagi chanbiba adu ngairingeida, nakhoi nasabu Tengban Mapugi nungsibada leiyu. (aiōnios )
kwa Mulungu yekhayo, Mpulumutsi wathu, kwa Iye kukhale ulemerero, ukulu, mphamvu ndi ulamuliro, mwa Yesu Khristu Ambuye athu, kuyambira isanayambe nthawi, tsopano mpaka muyaya. Ameni. (aiōn )
eikhoigi Kanbiba Mapu amatta ngairaba Tengban Mapua, eikhoigi Mapu Ibungo Jisu Christtagi mapanna matik mangal, chinglemba, panggal amasung matik houjik amadi matam pumnamakki oina leiba oirasanu! Amen. (aiōn )
ndipo watisandutsa mafumu ndi ansembe kuti tizitumikira Mulungu ndi Atate ake. Kwa Iye kukhale ulemerero ndi mphamvu ku nthawi zosatha, Ameni. (aiōn )
amasung Ibungogi Mapa Tengban Mapubu thougal toujanaba eikhoibu purohitsinggi ningthouleibak ama oihanbire. Jisu Christtagi maphamda matam pumnamakta matik mangal amadi pangal leiba oisanu! Amen. (aiōn )
Ine ndine Wamoyo; ndinali wakufa ndipo taona ndine wamoyo mpaka muyaya! Ndipo ndili ndi makiyi a imfa ndi Hade. (aiōn , Hadēs )
aduga eidi ahingba aduni, eihak sirure, adubu yeng-u houjikti ei lomba naida naidana hingle. Aduga eina asibagi amasung khamnung leibakki so adu pairi. (aiōn , Hadēs )
Nthawi zonse zamoyozo zimapereka ulemerero, ulemu ndi mayamiko kwa uja wokhala pa mpando waufumu, amene ali ndi moyo wamuyaya. (aiōn )
Thawaipanba mari aduna phambal adugi mathakta phamliba lomba naidana hingliba Ibungo adugi matik mangalgi, ikai khumnabagi amadi thagatpagi isei saklammi. Amasung makhoina asumna touba matamda, (aiōn )
Izi zikamachitika akuluakulu 24 aja amadzigwetsa pansi pamaso pa wokhala pa mpando waufumuyo, namupembedza wokhala ndi moyo wamuyayayo. Iwo amaponya pansi zipewa zawo zaufumu patsogolo pa mpando waufumu nati: (aiōn )
Ahal laman kunmari aduna phambaldugi mathakta phamliba Ibungo mahakki maangda tuthajaduna lomba naidana hingliba Ibungo mahakpu khurumjarammi. Makhoigi luhupsing adu phambaldugi mangda louthoktuna thamjaraga hai, (aiōn )
Kenaka ndinamva mawu a cholengedwa chilichonse kumwamba, pa dziko lapansi, kunsi kwa dziko lapansi, pa nyanja ndi zonse zili mʼmenemo zikuyimba kuti, “Kwa wokhala pa mpando waufumu ndi kwa Mwana Wankhosa, kukhale mayamiko, ulemu, ulemerero ndi mphamvu (aiōn )
Aduga swargada, malemda, malemgi leironungda amadi samudrada leiba thawai panba khudingmakna isei sakpa eina tare: Phambal aduda phamliba Ibungo mangonda amasung Yaomacha aduda, thagatpa, ikai khumnaba, matik mangal amasung touba ngamba matik adu, lomba naida naidana leiba oisanu. (aiōn )
Nditayangʼana patsogolo panga ndinaona kavalo wotuwa! Wokwerapo wake dzina lake linali Imfa ndipo Hade inali kumutsatira pambuyo pake. Anapatsidwa ulamuliro pa gawo limodzi la magawo anayi a dziko lapansi kuti aphe ndi lupanga, njala, mliri, ndi zirombo zakuthengo za mʼdziko lapansi. (Hadēs )
Aduga eina yengbada, maksinba machugi sagol ama eina ure. Madugi mathakta tongliba mahak adugi maming adu asiba kou-i aduga khamnung leibakna mahakki tung nakna illammi. Malemgi saruk mari thokpagi amagi mathakta lalna, chaktangbana, laina laichatna, amadi lamsasingna hatnaba makhoigi mathakta matik pire. (Hadēs )
Iwo anati, “Ameni! Matamando ndi ulemerero, nzeru, mayamiko, ulemu, ulamuliro ndi mphamvu zikhale kwa Mulungu wathu kunthawi zanthawi, Ameni!” (aiōn )
Hairak-i, “Amen! Thagat-khurumjaba, matik mangal, lousing, thagatchaba, ikai khumnaba, panggal, touba ngamba matik, lomba naidana naidana eikhoigi Tengban Mapugi oisanu! Amen!” (aiōn )
Mngelo wachisanu anayimba lipenga lake, ndipo ndinaona nyenyezi ikugwa pa dziko lapansi kuchokera ku thambo. Nyenyeziyo inapatsidwa kiyi ya ku chidzenje chakuya. (Abyssos )
Adudagi mangasuba swargadut aduna mahakki peresingga adu khongle amasung atiyadagi thawanmichak ama malemda tarakpa eina ure. Aduga mangonda makha naidaba komgi sow pire. (Abyssos )
Nyenyeziyo itatsekula pa chidzenje chakuyacho panatuluka utsi ngati wochokera mʼngʼanjo yayikulu. Dzuwa ndi thambo zinada chifukwa cha utsi ochokera mʼdzenjemo. (Abyssos )
Thawanmichak aduna makha naidaba kom adu hangdokle amasung achouba meiphamdagi meikhu thorakpagum madudagi meikhu thorakle, aduga makha naidaba komdagi thorakliba meikhu aduna numit amadi atiyabu mamhalle. (Abyssos )
Mfumu yawo inali mngelo wolamulira Chidzenje chakuya chija. Mʼchihebri dzina lake ndi Abadoni ndipo mʼChigriki ndi Apoliyoni (tanthauzo lake ndiye kuti, Wowononga). (Abyssos )
Makha naidaba kombu pannaba swargadut aduna makhoigi mathakta ningthou oina palli. Mahakki mamingdi Hebrew londa Abaddon kou-i; aduga Greek-tana Apollyon kou-i (wahandokti “Manghan takhanba mi” haibani). (Abyssos )
Mngeloyo analumbira mʼdzina la Iye wokhala ndi moyo mpaka muyaya, amene analenga kumwamba ndi zonse zili kumeneko, dziko lapansi ndi zonse zili mʼmenemo, nyanja ndi zonse zili mʼmenemo, nati, “Pasakhalenso zochedwa tsopano! (aiōn )
Aduga swarga, malem, samudra amasung maduda leiriba pumnamakpu sembiba, lomba naidana hingliba Tengban Mapugi mingda wasakladuna hairak-i, “Amuk Panthararoi.” (aiōn )
Tsono zikadzatsiriza umboni wawowo, chirombo chotuluka mʼChidzenje chakuya chija chidzachita nawo nkhondo nʼkuzigonjetsa mpaka kuzipha. (Abyssos )
Makhoina makhoigi sakhi piba loirabada, makha naidaba komdagi thorakpa sa aduna makhoigi maiyokta landagani. Amasung mahakna makhoibu maithiba piduna makhoibu hatkani. (Abyssos )
Mngelo wachisanu ndi chiwiri anawomba lipenga lake, ndipo kumwamba kunamveka mawu ofuwula amene anati, “Ufumu wa dziko lapansi uli mʼmanja mwa Ambuye athu ndi Khristu wake uja, ndipo adzalamulira mpaka muyaya.” (aiōn )
Adudagi taretsuba swargadut aduna mahakki peresingga adu khongle, aduga swargada ahouba khonjelsingda hairak-i, “Taibangpanbagi ningthouleibak adu eikhoigi Ibungogi amadi mahakki Messiah-gi oirakle, aduga mahakna lomba naida naidana pangani” (aiōn )
Kenaka ndinaona mngelo wina akuwuluka mu mlengalenga ndipo anali ndi Uthenga Wabwino wamuyaya woti akalalikire kwa anthu okhala pa dziko lapansi, kwa a mtundu uliwonse, a fuko lililonse, a chiyankhulo chilichonse ndi kwa anthu onse. (aiōnios )
Adudagi eina malemda leiriba misingda, mi kanglup khuding, salai khuding, lol khuding amadi phurup khudingda laothoknaba aphaba paogi lomnaidaba paojelga loinana awangba atiyada pairiba atoppa swargadut ama eina ure. (aiōnios )
Ndipo utsi wa moto wowazunzawo udzakwera kumwamba mpaka muyaya. Sikudzakhala kupumula usana ndi usiku kwa amene anapembedza chirombo chija ndi fano lake kapena kwa aliyense amene analembedwa chizindikiro cha dzina lake lija.” (aiōn )
Makhoida awaba piriba meigi meikhu adu lomba naida naidana mathakta kakhatkani. Aduga sa adubu amadi magi murti adubu khurumbasing amasung mahakki minggi khudam phangba makhoising adugi awaba adu ahing nungthil anida leppa nairoi.” (aiōn )
Ndipo kenaka chimodzi cha zamoyo zinayi zija chinapereka kwa angelo asanu ndi awiri mbale zisanu ndi ziwiri zodzaza ndi ukali wa Mulungu amene ali ndi moyo mpaka muyaya. (aiōn )
Thawaipanba mari adudagi amana swargadut taret aduda lomba naidana hingduna leiriba Tengban Mapugi meihouna saobana thallaba sanagi tenggot taret adu pirammi. (aiōn )
Chirombo chimene wachionachi chinalipo kale koma tsopano kulibe ndipo chidzatuluka ku chidzenje chakuya ndi kupita kukawonongedwa. Anthu okhala pa dziko lapansi amene mayina awo sanalembedwe mʼbuku lamoyo kuyambira pa kulengedwa kwa dziko lapansi adzadabwa pamene adzaona chirombocho, chifukwa chinalipo kale, tsopano kulibe, komabe chidzabwera. (Abyssos )
Nangna uriba sa asi matam amada leirammi, adubu mahak houjikti leitre; adumakpu mahak makha naidaba kom adudagi amuk kakhatlakkadouri aduga mahakki mang-takphamda chatkani. Taibangpan semdringei mamangdagi hingbagi lairikta makhoigi ming isinkhidaba malemda leibasingna sa adubu uba matamda ngakkani, maramdi mahakna matam amada leirammi, houjikna leitre adumakpu amuk lakkadouri. (Abyssos )
Ndipo anafuwulanso kuti, “Haleluya! Utsi wochokera kwa mkazi wadamayo udzakwera kumwamba mpaka muyaya.” (aiōn )
Aduga makhoina amuk hanna laorak-i: “Halleluya! Achouba sahar adu chakthekpagi meiridagi thorakpa meikhuna lomba naida naidana ka-khatli.” (aiōn )
Koma chirombocho chinagwidwa pamodzi ndi mneneri wonyenga uja amene anachita zizindikiro zodabwitsa pamaso pake. Ndi zizindikirozi anasocheretsa amene analembedwa chizindikiro cha chirombocho napembedza fano lake. Onse awiri anaponyedwa amoyo mʼnyanja yamoto yasulufule wotentha. (Limnē Pyr )
Adubu sa aduga loinana mahakki mamangda angakpa thabak toukhiba Tengban Mapugi wa takthoksinaba mi aduga punna phare. (Mahakna sa adugi khudam leiba amadi sa adugi murtibu khurumba makhoising adubu minamkhiba adu angakpa thabaksing asigi mapannani.) Sa amadi Tengban Mapugi wa takthoksinnaba animakpu kantrukna chakliba meigi pat aduda hingna hunthare. (Limnē Pyr )
Ndipo ndinaona mngelo akutsika kuchokera kumwamba ali ndi kiyi ya ku chidzenje chakuya chija atanyamula mʼdzanja lake unyolo waukulu. (Abyssos )
Adudagi swargadut amana makha naidaba komgi so amasung chaoraba yotling phalang paiduna swargadagi kumtharakpa eina ure. (Abyssos )
Anamuponya ku chidzenje chakuya chija namutsekera ndi kiyi ndi kumatirira pa khomopo kuti asatulukenso kukanyenga mitundu ya anthu mpaka patapita zaka 1,000. Zikadzatha zakazo, adzamumasula kwa kanthawi pangʼono chabe. (Abyssos )
Chahi lising amadu loidriba phaoba phurupsingbu amuk hanna minamba ngamdanaba swargadut aduna mahakpu makha naidaba komda hunjille aduga so lonsinduna chum namduna thamkhi. Madugi matungda mahakpu matam khradanggi oina thadokpa tai. (Abyssos )
Ndipo Mdierekezi amene anawanyenga, anaponyedwa mʼnyanja ya sulufule wotentha, kumene kunaponyedwa chirombo chija ndi mneneri wonama uja. Iwo adzazunzika usiku ndi usana kwamuyaya. (aiōn , Limnē Pyr )
Adudagi makhoibu minamkhiba Devil adubu sa amadi Tengban Mapugi wa takthoksinaba adubu hanna hunthakhraba mei amadi kantrukki pat aduda hunthare; aduga makhoibu ahing nungthil lomba naida naidana awa meichak khanghangani. (aiōn , Limnē Pyr )
Nyanja inapereka amene anaferamo ndipo imfa ndi Hade zinapereka akufa ake ndipo munthu aliyense anaweruzidwa monga mwa ntchito zake. (Hadēs )
Adudagi samudrana magi manungda leiriba asibasingbu pithokle. Aduga siba amadi khamnung leibaknasu makhoigi manungda leiriba asibasingbu pithokle. Amasung makhoi pumnamakpu makhoi makhoina toukhiba thabakki matung-inna wayelle. (Hadēs )
Kenaka imfa ndi Hade zinaponyedwa mʼnyanja ya moto. Nyanja yamoto ndiyo imfa yachiwiri. (Hadēs , Limnē Pyr )
Adudagi siba amadi khamnung leibakpu meigi pat manungda langsille. Meigi pat asi anisuba siba aduni. (Hadēs , Limnē Pyr )
Ngati dzina la wina aliyense silinapezeke mʼBuku Lamoyo, anaponyedwa mʼnyanja yamoto. (Limnē Pyr )
Hingbagi lairikta makhoigi ming isinba phangdaba makhoising adubu meigi pat aduda hunjille. (Limnē Pyr )
Koma amantha, osakhulupirira, okonda zonyansa, opha anthu, achiwerewere, amatsenga, opembedza mafano ndi abodza, malo awo adzakhala nyanja yamoto ya sulufule wotentha. Iyi ndi imfa yachiwiri.” (Limnē Pyr )
Adubu pangdabasing, thajadabasing, tukkachaningai oibasing, mihatpasing, nupa nupi lannabasing, hidam yaidambagi thabak toubasing, lai murti latpasing amasung chinthiba pumnamakki panthungdi achakpa kantrukki meigi pat aduda oigani. Masi anisuba siba aduni.” (Limnē Pyr )
Sipadzakhalanso usiku. Sadzafuna kuwala kwa nyale kapena kwa dzuwa pakuti Ambuye Mulungu adzakhala kuwala kwawo. Ndipo adzalamulira kwamuyaya. (aiōn )
Mapham aduda ahing amuk leiraroi, aduga makhoina thaomei amasung numitki mangalsu mathou tararoi, maramdi Ibungo Tengban Mapuna makhoigi mangal oigani; aduga makhoina ningthougumna lomba naida naidana pangani. (aiōn )