< Nehemiya 7 >
1 Khoma linamangidwa ndipo zitseko zinayikidwa. Pambuyo pake alonda a Nyumba ya Mulungu, oyimba nyimbo ndiponso Alevi anasankhidwa.
Surların onarımı bitip kapılar yerine takıldıktan sonra, kapı nöbetçileri, ezgiciler ve Levililer göreve atandı.
2 Kenaka ine ndinasankha mʼbale wanga Hanani pamodzi ndi Hananiya woyangʼanira nsanja yankhondo kukhala olamulira Yerusalemu chifukwa iyeyu anali munthu odalirika ndi woopa Mulungu kuposa anthu ena.
Kardeşim Hanani'yle kale komutanı Hananya'yı Yeruşalim'e yönetici atadım. Hananya güvenilir bir kişiydi. Çoğu insandan daha çok Tanrı'dan korkardı.
3 Ine ndinawawuza kuti, “Musalole kuti zipata za Yerusalemu zitsekulidwe mpaka dzuwa litatentha, ndipo alonda asanaweruke aonetsetse kuti atseka zitseko ndi kuzipiringidza. Musankhe alonda pakati pa anthu okhala mu Yerusalemu, ena akhale pa malo pawo ndi ena akhale moyangʼanana ndi nyumba zawo.”
Onlara, “Güneş ortalığı ısıtıncaya kadar Yeruşalim kapıları açılmasın” dedim, “Kapı nöbetçileri görev başındayken kapıları kapalı tutsunlar. Kapıları siz sürgüleyin ve Yeruşalim'de oturanlara nöbet görevi verin. Bazıları bu görevi yapsın, bazıları da evlerinin çevresinde nöbet tutsun.”
4 Tsono mzinda wa Yerusalemu unali wotambasuka ndiponso waukulu koma munali anthu ochepa ndipo nyumba zinali zisanamangidwe.
Yeruşalim geniş, büyük bir kentti, ama nüfusu azdı. İçindeki evler henüz onarılmamıştı.
5 Ndipo Mulungu wanga anayika mu mtima mwanga maganizo oti ndisonkhanitse anthu olemekezeka, akuluakulu ndi anthu onse kuti alembetse mayina mwa mabanja awo. Ndinapeza buku limene munalembedwa mayina a mabanja a iwo amene anayamba kubwera kuchokera ku ukapolo. Izi ndi zimene ndinazipeza zitalembedwa mʼmenemo:
Tanrım soylarına göre halkın sayımı yapılabilsin diye soyluları, yetkilileri ve bütün halkı toplamamı istedi. Sürgünden ilk dönenlerin soy kütüğünü buldum. İçinde şunlar yazılıydı:
6 Awa ndi anthu a mʼchigawo cha Yuda amene anabwerera kuchokera ku ukapolo amene Nebukadinezara mfumu ya Babuloni anawatenga ukapolo. Iwo anabwerera ku Yerusalemu ndi ku Yuda, aliyense ku mzinda wa makolo ake.
Babil Kralı Nebukadnessar'ın sürgün ettiği insanlar yaşadıkları ilden Yeruşalim ve Yahuda'daki kendi kentlerine döndü.
7 Anabwera pamodzi ndi atsogoleri awa: Zerubabeli, Yesuwa, Nehemiya, Azariya, Raamiya, Nahamani, Mordekai, Bilisani, Misipereti, Bigivai, Nehumu ndi Baana. Tsono chiwerengero cha anthu a ku Israeli chinali chotere:
Bunlar Zerubbabil, Yeşu, Nehemya, Azarya, Raamya, Nahamani, Mordekay, Bilşan, Misperet, Bigvay, Nehum ve Baana'nın önderliğinde geldiler. Sürgünden dönen İsrailliler'in sayıları şöyleydi:
8 Zidzukulu za Parosi 2,172
Paroşoğulları: 2 172
9 Zidzukulu za Sefatiya 372
Şefatyaoğulları: 372
11 Zidzukulu za Pahati-Mowabu (kudzera mu mʼbado wa Yesuwa ndi Yowabu) 2,818
Yeşu ve Yoav soyundan Pahat-Moavoğulları: 2 818
12 Zidzukulu za Elamu 1,254
Elamoğulları: 1 254
14 Zidzukulu za Zakai 760
Zakkayoğulları: 760
15 Zidzukulu za Binuyi 648
Binnuyoğulları: 648
16 Zidzukulu za Bebai 628
Bevayoğulları: 628
17 Zidzukulu za Azigadi 2,322
Azgatoğulları: 2 322
18 Zidzukulu za Adonikamu 667
Adonikamoğulları: 667
19 Zidzukulu za Abigivai 2,067
Bigvayoğulları: 2067
20 Zidzukulu za Adini 655
Adinoğulları: 655
21 Zidzukulu za Ateri (kudzera mwa Hezekiya) 98
Hizkiya soyundan Ateroğulları: 98
22 Zidzukulu za Hasumu 328
Haşumoğulları: 328
23 Zidzukulu za Bezayi 324
Besayoğulları: 324
24 Zidzukulu za Harifu 112
Harifoğulları: 112
25 Zidzukulu za Gibiyoni 95.
Givonlular: 95
26 Anthu a ku Betelehemu ndi Netofa 188
Beytlehemliler ve Netofalılar: 188
27 Anthu a ku Anatoti 128
Anatotlular: 128
28 Anthu a ku Beti-Azimaveti 42
Beytazmavetliler: 42
29 Anthu a ku Kiriati Yeyarimu Kefira ndi Beeroti 743
Kiryat-Yearimliler, Kefiralılar ve Beerotlular: 743
30 Anthu a ku Rama ndi Geba 621
Ramalılar ve Gevalılar: 621
31 Anthu a ku Mikimasi 122
Mikmaslılar: 122
32 Anthu a ku Beteli ndi Ai 123
Beytel ve Ay kentlerinden olanlar: 123
33 Anthu a ku Nebo winayo 52
Öbür Nevo Kenti'nden olanlar: 52
34 Ana a Elamu wina 1,254
Öbür Elam Kenti'nden olanlar: 1254
35 Zidzukulu za Harimu 320
Harimliler: 320
36 Zidzukulu za Yeriko 345
Erihalılar: 345
37 Zidzukulu za Lodi, Hadidi ndi Ono 721
Lod, Hadit ve Ono kentlerinden olanlar: 721
38 Zidzukulu za Senaya 3,930.
Senaalılar: 3 930
39 Ansembe anali awa: A banja la Yedaya (ndiye kuti zidzukulu za Yesuwa) 973
Kâhinler: Yeşu soyundan Yedayaoğulları: 973
40 Zidzukulu za Imeri 1,052
İmmeroğulları: 1 052
41 Zidzukulu za Pasi-Huri 1,247
Paşhuroğulları: 1 247
42 Zidzukulu za Harimu 1,017.
Harimoğulları: 1017
43 Alevi anali awa: A banja la Yesuwa ndi Kadimieli, ndiye kuti zidzukulu za Hodaviya 74.
Levililer: Kadmiel ve Hodeva soyundan gelen Yeşuoğulları: 74
44 Anthu oyimba: Zidzukulu za Asafu 148.
Ezgiciler: Asafoğulları: 148
45 Alonda a ku Nyumba ya Mulungu anali awa: Zidzukulu za Salumu, Ateri, Talimoni, Hatita ndi Sobai 138.
Tapınak kapı nöbetçileri: Şallumoğulları, Ateroğulları, Talmonoğulları, Akkuvoğulları, Hatitaoğulları, Şovayoğulları: 138
46 Anthu ogwira ntchito ku Nyumba ya Mulungu anali awa: Zidzukulu za Ziha, zidzukulu za Hasufa, zidzukulu za Tabaoti,
Tapınak görevlileri: Sihaoğulları, Hasufaoğulları, Tabbaotoğulları,
47 Zidzukulu Kerosi, zidzukulu za Siya, zidzukulu za Padoni
Kerosoğulları, Siaoğulları, Padonoğulları,
48 Zidzukulu za Lebana za Hagaba, ndi za Salimayi,
Levanaoğulları, Hagavaoğulları, Şalmayoğulları,
49 Zidzukulu za Hanani, zidzukulu za Gideli, zidzukulu za Gahari,
Hananoğulları, Giddeloğulları, Gaharoğulları,
50 Zidzukulu za Reyaya, zidzukulu za Rezini, zidzukulu za Nehoda,
Reayaoğulları, Resinoğulları, Nekodaoğulları,
51 Zidzukulu za Gazamu, zidzukulu za Uza, zidzukulu za Paseya,
Gazzamoğulları, Uzzaoğulları, Paseahoğulları,
52 Zidzukulu za Besai, zidzukulu za Meunimu, zidzukulu za Nefusimu,
Besayoğulları, Meunimoğulları, Nefişesimoğulları,
53 Zidzukulu za Bakibuku, zidzukulu za Hakufa, zidzukulu za Harihuri,
Bakbukoğulları, Hakufaoğulları, Harhuroğulları,
54 Zidzukulu za Baziliti, zidzukulu za Mehida, zidzukulu za Harisa,
Baslitoğulları, Mehidaoğulları, Harşaoğulları,
55 Zidzukulu za Barikosi, zidzukulu za Sisera, zidzukulu za Tema
Barkosoğulları, Siseraoğulları, Temahoğulları,
56 Zidzukulu za Neziya, ndi zidzukulu za Hatifa.
Nesiahoğulları, Hatifaoğulları.
57 Zidzukulu za antchito a Solomoni: Zidzukulu za Sotai, zidzukulu za Sofereti, zidzukulu za Perida
Süleyman'ın kullarının soyu: Sotayoğulları, Soferetoğulları, Peridaoğulları,
58 zidzukulu za Yaala, zidzukulu za Darikoni, zidzukulu za Gideli,
Yalaoğulları, Darkonoğulları, Giddeloğulları,
59 zidzukulu za Sefatiya, zidzukulu za Hatilu zidzukulu za Pokereti-Hazebaimu ndi zidzukulu Amoni.
Şefatyaoğulları, Hattiloğulları, Pokeret-Hassevayimoğulları, Amonoğulları.
60 Anthu onse ogwira ntchito ku Nyumba ya Mulungu pamodzi ndi zidzukulu za antchito a Solomoni analipo 392.
Tapınak görevlileriyle Süleyman'ın kullarının soyundan olanlar: 392
61 Ali munsiwa anachokera ku Teli-Mela, Teri-Harisa, Kerubi, Adoni, ndi Imeri, koma sanathe kunena mwa tchutchutchu kuti makolo awo kapena mafuko awo analidi Aisraeli kapena ayi.
Tel-Melah, Tel-Harşa, Keruv, Addon ve İmmer'den dönen, ancak hangi aileden olduklarını ve soylarının İsrail'den geldiğini kanıtlayamayanlar şunlardır:
62 Zidzukulu za Delaya, zidzukulu za Tobiya ndi zidzukulu za Nekoda 642.
Delayaoğulları, Toviyaoğulları, Nekodaoğulları: 642
63 Ndiponso ena pakati pa ansembe anali awa: zidzukulu za Hobiya, zidzukulu za Hakozi ndi zidzukulu za Barizilai (munthu amene anakwatira mwana wamkazi wa Barizilai wa ku Giliyadi ndipo amatchedwa dzina limenelo).
Kâhinlerin soyundan: Hovayaoğulları, Hakkosoğulları ve Gilatlı Barzillay'ın kızlarından biriyle evlenip kayınbabasının adını alan Barzillay'ın oğulları.
64 Iwowa anafufuzafufuza mayina awo mʼbuku la mibado ya mabanja awo ndipo sanapeze mayina awo kotero anachotsedwa pa unsembe nawerengedwa ngati odetsedwa pa chipembedzo.
Bunlar soy kütüklerini aradılar. Ama yazılı bir kayıt bulamayınca, kâhinlik görevi ellerinden alındı.
65 Choncho bwanamkubwa anawawuza anthuwo kuti asamadye nawo chakudya china chilichonse choperekedwa kwa Mulungu mpaka patapezeka wansembe wodziwa kugwiritsa bwino ntchito ya Urimu ndi Tumimu.
Vali, Urim ile Tummim'i kullanan bir kâhin çıkıncaya dek en kutsal yiyeceklerden yememelerini buyurdu.
66 Chiwerengero chonse cha anthuwa chinali 42,360.
Bütün halk toplam 42 360 kişiydi.
67 Kuwonjezera pamenepa panali antchito awo aamuna ndi aakazi 7,337 ndiponso anthu aamuna ndi aakazi oyimba nyimbo okwanira 245.
Ayrıca 7 337 erkek ve kadın köle, kadınlı erkekli 245 ezgici, 736 at, 245 katır, 435 deve, 6 720 eşek vardı.
68 Panali akavalo 736, abulu angʼonoangʼono 245.
69 Ngamira zawo zinalipo 435 ndipo abulu analipo 6,720.
70 Atsogoleri ena a mabanja anapereka mphatso zothandizira ntchito. Bwanamkubwa anapereka ku thumba losungira chuma, ndalama zagolide za makilogalamu asanu ndi atatu, mabeseni makumi asanu ndi zovala za ansembe 530.
Bazı aile başları onarım işi için bağışta bulundu: Vali hazineye 1 000 darik altın, 50 çanak, 530 kâhin mintanı bağışladı.
71 Atsogoleri ena amabanja anapereka ku thumba losungira chuma ndalama zagolide zokwana makilogalamu 168, ndiponso ndalama za siliva zokwana makilogalamu 1,250.
Bazı aile başları da iş için hazineye 20 000 darik altın, 2 200 mina gümüş verdiler.
72 Anthu ena onse otsala anapereka ndalama zagolide zokwana makilogalamu 168, ndalama za siliva zokwana makilogalamu 140, ndiponso zovala za ansembe 67.
Halkın geri kalanı ise, toplam 20 000 darik altın, 2 000 mina gümüş ve 67 kâhin mintanı verdi.
73 Choncho ansembe, Alevi, alonda a Nyumba ya Mulungu, anthu oyimba nyimbo, ena mwa anthu wamba, ogwira ntchito ku Nyumba ya Mulungu pamodzi ndi Aisraeli ena onse ankakhala mʼmizinda yawo. Pofika mwezi wachisanu ndi chiwiri Aisraeli onse anali atakhazikika mʼmizinda yawo.
Kâhinler, Levililer, tapınak görevlileri ve kapı nöbetçileri, ezgiciler, sıradan insanlar ve bütün İsrailliler kentlerine yerleştiler.