< Nehemiya 7 >
1 Khoma linamangidwa ndipo zitseko zinayikidwa. Pambuyo pake alonda a Nyumba ya Mulungu, oyimba nyimbo ndiponso Alevi anasankhidwa.
Ie nifonitse i kijoliy naho fa natroako o lalañeo naho fa tinendreko o mpañambeñeo naho o mpisaboo vaho o nte-Levio,
2 Kenaka ine ndinasankha mʼbale wanga Hanani pamodzi ndi Hananiya woyangʼanira nsanja yankhondo kukhala olamulira Yerusalemu chifukwa iyeyu anali munthu odalirika ndi woopa Mulungu kuposa anthu ena.
le nafantoko amy Kananý, rahalahiko naho amy Kananià, mpifelek’ i anjombam-panjakay ty fandiliañe Ierosalaime (amy te ondaty vañon-dre, nañeveñe aman’ Añahare mandikoatse i màroy);
3 Ine ndinawawuza kuti, “Musalole kuti zipata za Yerusalemu zitsekulidwe mpaka dzuwa litatentha, ndipo alonda asanaweruke aonetsetse kuti atseka zitseko ndi kuzipiringidza. Musankhe alonda pakati pa anthu okhala mu Yerusalemu, ena akhale pa malo pawo ndi ena akhale moyangʼanana ndi nyumba zawo.”
le nanoako ty hoe: Ko sokafe’ areo o lalambei’ Ierosalaimeo ampara’ te mafana-voho ndra te eo o mpigaritseo, arindrino naho agabeño; vaho joboño mpañambeñe amo mpimone’ Ierosalaimeo, songa ami’ty fiambena’e naho sindre tandrife’ i anjomba’ey.
4 Tsono mzinda wa Yerusalemu unali wotambasuka ndiponso waukulu koma munali anthu ochepa ndipo nyumba zinali zisanamangidwe.
Toe bey naho jabajaba o rovao fe tsy niampeampe t’indaty ao vaho mboe tsy namboareñe o anjombao.
5 Ndipo Mulungu wanga anayika mu mtima mwanga maganizo oti ndisonkhanitse anthu olemekezeka, akuluakulu ndi anthu onse kuti alembetse mayina mwa mabanja awo. Ndinapeza buku limene munalembedwa mayina a mabanja a iwo amene anayamba kubwera kuchokera ku ukapolo. Izi ndi zimene ndinazipeza zitalembedwa mʼmenemo:
Le najon’ Añahareko an-troko ao ty hanontoñe o mpiaoloo naho o mpifehe ondatio, hampiantoñoñe iereo. Le nitreako ty bokem-piantoño’ o nionjoñe mb’atoy tam-baloha’e vaho nizoeko sinokitse ao ty hoe:
6 Awa ndi anthu a mʼchigawo cha Yuda amene anabwerera kuchokera ku ukapolo amene Nebukadinezara mfumu ya Babuloni anawatenga ukapolo. Iwo anabwerera ku Yerusalemu ndi ku Yuda, aliyense ku mzinda wa makolo ake.
Zao o ana’ i borizà niavotse am-pandrohizañe amo nasese mb’eoo, amo nasese’ i Nebokadnetsare mpanjaka’ i Baveleo vaho nimpoly mb’e Ierosalaime naho Iehoda añe, songa mb’an-drova’e mb’eo;
7 Anabwera pamodzi ndi atsogoleri awa: Zerubabeli, Yesuwa, Nehemiya, Azariya, Raamiya, Nahamani, Mordekai, Bilisani, Misipereti, Bigivai, Nehumu ndi Baana. Tsono chiwerengero cha anthu a ku Israeli chinali chotere:
o nindre amy Zerobabele mb’ etoao, Iesoa, i Nekemià, i Atsarià, i Raamià, i Nahamanià, i Mordekay, i Bilsane, i Misperete, i Bigvay, i Nekome, i Baanà. Ty ia’ ty lahilahy amo nte-Israeleo, le zao:
8 Zidzukulu za Parosi 2,172
O ana’ i Paroseo, roarivo-tsi-zato-tsi-fitompolo-ro’amby.
9 Zidzukulu za Sefatiya 372
O ana’ i Sefatiào: telonjato-tsi-fitompolo-ro’amby.
O ana’ i Arào, enenjato-tsi-limampolo-ro’amby.
11 Zidzukulu za Pahati-Mowabu (kudzera mu mʼbado wa Yesuwa ndi Yowabu) 2,818
O ana’ i Pakate-moabeo, o ana’ Iesoào naho Ioabeo, ro’arivo-tsi-valonjato-tsi-folo-valo’amby.
12 Zidzukulu za Elamu 1,254
O ana’ i Elameo, arivo-tsi-roanjato-tsi-limampolo-efats’amby.
O ana’ i Zatòo, valonjato-tsi-efapolo-lim’ amby.
14 Zidzukulu za Zakai 760
O ana’ i Zakaio, fitonjato-tsi-enempolo.
15 Zidzukulu za Binuyi 648
O ana’ i Binoio, enenjato-tsi-efapolo-valo’ amby.
16 Zidzukulu za Bebai 628
O ana’ i Bebaio, enenjato-tsi-roapolo-valo’ amby.
17 Zidzukulu za Azigadi 2,322
O ana’ i Azgadeo: roarivo-tsi-telonjato-tsi-roapolo-ro’amby.
18 Zidzukulu za Adonikamu 667
O ana’ i Adonikameo, enen-jato-tsi-enempolo-fito’ amby.
19 Zidzukulu za Abigivai 2,067
O ana’ i Bigaio, ro’arivo-tsi-enempolo-fito’ amby.
20 Zidzukulu za Adini 655
O ana’ i Adineo, enenjato-tsi-limampolo-lim’ amby.
21 Zidzukulu za Ateri (kudzera mwa Hezekiya) 98
O ana’ i Atere Kizkiào, sivampolo-valo’ amby.
22 Zidzukulu za Hasumu 328
O ana’ i Kasomeo, telonjato-tsi-roapolo-valo’ amby.
23 Zidzukulu za Bezayi 324
O ana’ i Betsaio, telonjato-tsi-roapolo-efats’ amby.
24 Zidzukulu za Harifu 112
O ana’ i Karifeo, zato-tsi-folo-ro’amby.
25 Zidzukulu za Gibiyoni 95.
O ana’ i Giboneo, sivampolo-lim’ amby.
26 Anthu a ku Betelehemu ndi Netofa 188
O nte-Betlekheme naho i Netofào, zato-tsi-valopolo-valo’amby.
27 Anthu a ku Anatoti 128
O nte-Anatoteo, zato-tsi-roapolo-valo’ amby,
28 Anthu a ku Beti-Azimaveti 42
O nte-Bete-azemaveteo, efapolo-ro’ amby.
29 Anthu a ku Kiriati Yeyarimu Kefira ndi Beeroti 743
O nte-Kiriate-Iearimeo, i Kefirà vaho i Beroteo, fiton-jato-tsi-efapolo-telo’ amby.
30 Anthu a ku Rama ndi Geba 621
O nte-Ramà naho nte-Gebao, enen-jato-tsi-roapolo-raik’ amby.
31 Anthu a ku Mikimasi 122
O nte-Mikmaseo, zato-tsi-roapolo-ro’ amby.
32 Anthu a ku Beteli ndi Ai 123
O nte Betele naho Aio, zato-tsi-roapolo-telo’amby.
33 Anthu a ku Nebo winayo 52
O nte-Nebo ila’eo, limampolo-ro’ amby.
34 Ana a Elamu wina 1,254
O ana’ i Elame ila’eo, arivo-tsi-roanjato-tsi-limampolo-efats’amby.
35 Zidzukulu za Harimu 320
O ana’ i Karimeo, telonjato-tsi-roapolo.
36 Zidzukulu za Yeriko 345
O ana’ Ierikoo, telonjato-tsi-efapolo-lim’ amby.
37 Zidzukulu za Lodi, Hadidi ndi Ono 721
O ana’ i Lodeo, i Kadide vaho i Ono, fitonjato-tsi-roapolo-raik’amby.
38 Zidzukulu za Senaya 3,930.
O ana’ i Senàao, teloarivo-tsi-sivanjato-tsi-telopolo.
39 Ansembe anali awa: A banja la Yedaya (ndiye kuti zidzukulu za Yesuwa) 973
O mpisoroñeo: o ana’ Ikedaià, tañ’ anjomba’ Iesoào, sivanjato-tsi-fitom-polo-telo’ amby.
40 Zidzukulu za Imeri 1,052
O ana’ Imereo, arivo-tsi-limampolo-ro’amby.
41 Zidzukulu za Pasi-Huri 1,247
O ana’ i Pasoreo, arivo-tsi-roanjato-tsi-efapolo-fito’amby.
42 Zidzukulu za Harimu 1,017.
O ana’ i Karimeo, arivo-tsi-folo-fito’ amby.
43 Alevi anali awa: A banja la Yesuwa ndi Kadimieli, ndiye kuti zidzukulu za Hodaviya 74.
O nte-Levio: o ana’ Iesoao, a i Kadmieleo vaho o ana’ i Hodevào, fitom-polo-efats’amby.
44 Anthu oyimba: Zidzukulu za Asafu 148.
O mpisaboo: o ana’ i Asafeo, zato-tsi-efapolo-valo’ amby.
45 Alonda a ku Nyumba ya Mulungu anali awa: Zidzukulu za Salumu, Ateri, Talimoni, Hatita ndi Sobai 138.
O mpañambeñeo: o ana’ i Salomeo, o ana’ i Atereo, o ana’ i Talmoneo, o ana’ i Akobeo, o ana’ i Katitào, o ana’ i Sobaio, zato-tsi-telopolo-valo’amby.
46 Anthu ogwira ntchito ku Nyumba ya Mulungu anali awa: Zidzukulu za Ziha, zidzukulu za Hasufa, zidzukulu za Tabaoti,
O mpitoroñe amy anjombaio: o ana’ i Tsikào, o ana’ i Kasofào, o ana’ i Tabaoteo,
47 Zidzukulu Kerosi, zidzukulu za Siya, zidzukulu za Padoni
o ana’ i Keroseo, o ana’ i Siào, o ana’ i Padoneo,
48 Zidzukulu za Lebana za Hagaba, ndi za Salimayi,
o ana’ i Lebanao, o ana’ i Kagabào, o ana’ i Salmaio,
49 Zidzukulu za Hanani, zidzukulu za Gideli, zidzukulu za Gahari,
o ana’ i Kanàneo, o ana’ i Gideleo, o ana’ i Gakhareo,
50 Zidzukulu za Reyaya, zidzukulu za Rezini, zidzukulu za Nehoda,
o ana’ i Reaiào, o ana’ i Retsineo, o ana’ i Nekodao,
51 Zidzukulu za Gazamu, zidzukulu za Uza, zidzukulu za Paseya,
o ana’ i Gazameo, o ana’ i Ozào, o ana’ i Paseakeo,
52 Zidzukulu za Besai, zidzukulu za Meunimu, zidzukulu za Nefusimu,
o ana’ i Besaio, o ana’ i Meonimeo, o ana’ i Nefisesimeo
53 Zidzukulu za Bakibuku, zidzukulu za Hakufa, zidzukulu za Harihuri,
o ana’ i Bakokeo, o ana’ i Kakofào, o ana’ i Karkoreo,
54 Zidzukulu za Baziliti, zidzukulu za Mehida, zidzukulu za Harisa,
o ana’ i Batsliteo, o ana’ i Mekidào, o ana’ i Karsào,
55 Zidzukulu za Barikosi, zidzukulu za Sisera, zidzukulu za Tema
o ana’ i Barkoseo, o ana’ i Siserao, o ana’ i Tamakeo,
56 Zidzukulu za Neziya, ndi zidzukulu za Hatifa.
o ana’ i Netsiakeo, o ana’ i Katifào.
57 Zidzukulu za antchito a Solomoni: Zidzukulu za Sotai, zidzukulu za Sofereti, zidzukulu za Perida
O anam-pitoro’ i Selomòo: o ana’ i Sotahio, o ana’ i Sofereteo, o ana’ i Peridao,
58 zidzukulu za Yaala, zidzukulu za Darikoni, zidzukulu za Gideli,
o ana’ Ia’alào, o ana’ i Darkoneo, o ana’ i Gidelo,
59 zidzukulu za Sefatiya, zidzukulu za Hatilu zidzukulu za Pokereti-Hazebaimu ndi zidzukulu Amoni.
o ana’ i Sefatiào, o ana’i Katileo, o ana’ i Pokerete Hatsebaimeo, o ana’ i Amoneo.
60 Anthu onse ogwira ntchito ku Nyumba ya Mulungu pamodzi ndi zidzukulu za antchito a Solomoni analipo 392.
O hene mpitoron’ anjombao naho o anam-pitoro’ i Selomòo: telonjato-tsi-sivampolo-ro’ amby.
61 Ali munsiwa anachokera ku Teli-Mela, Teri-Harisa, Kerubi, Adoni, ndi Imeri, koma sanathe kunena mwa tchutchutchu kuti makolo awo kapena mafuko awo analidi Aisraeli kapena ayi.
Iretoañe ty niboak’e Tel-melà, i Tel-karsà, i Kerobe, i Adone vaho Imere: fe tsy nahafitoñoñe ty anjomban-droae’e ndra ty maha-tariratse iareo, ke t’ie nte-Israele:
62 Zidzukulu za Delaya, zidzukulu za Tobiya ndi zidzukulu za Nekoda 642.
O ana’ i Delaiào, o ana’ i Tobiào, o ana’ i Nekodao: enenjato-tsi-efapolo-ro’ amby.
63 Ndiponso ena pakati pa ansembe anali awa: zidzukulu za Hobiya, zidzukulu za Hakozi ndi zidzukulu za Barizilai (munthu amene anakwatira mwana wamkazi wa Barizilai wa ku Giliyadi ndipo amatchedwa dzina limenelo).
Le amo mpisoroñeo: o ana’ i Kabaiao, o ana’ i Hakotseo, o ana’ i Barzilao i nañenga ty raik’ amo anak’ ampela’ i Barzialy nte-Giladeo ho vali’ey le nitokaveñe ami’ty tahina’ iareo.
64 Iwowa anafufuzafufuza mayina awo mʼbuku la mibado ya mabanja awo ndipo sanapeze mayina awo kotero anachotsedwa pa unsembe nawerengedwa ngati odetsedwa pa chipembedzo.
Pinay amo sinokitse am-piantoñoñeo iareo fe tsy nahaisake; aa le natao ho maleotse vaho nasitak’ amy fisoroñañey.
65 Choncho bwanamkubwa anawawuza anthuwo kuti asamadye nawo chakudya china chilichonse choperekedwa kwa Mulungu mpaka patapezeka wansembe wodziwa kugwiritsa bwino ntchito ya Urimu ndi Tumimu.
Le hoe ty nanoa’ i Tirsatà, t’ie tsy hikama o miava-do’eo ampara’ te eo ty mpisoroñe hiongake reketse Orime naho Tomime.
66 Chiwerengero chonse cha anthuwa chinali 42,360.
Ty fitonto’ i valobohòke zay le efats’ ale-tsi-ro’ arivo-tsi-telonjato-tsi-enempolo,
67 Kuwonjezera pamenepa panali antchito awo aamuna ndi aakazi 7,337 ndiponso anthu aamuna ndi aakazi oyimba nyimbo okwanira 245.
mandikoatse o fetrek’ oro’eo naho o anak’ ampata’eo, le fito-arivo-tsi-telonjato-tsi-telopolo-fito’amby; naho am’ iereo ty lahilahy naho rakemba mpisabo roanjato-tsi-efapolo-lim’ amby.
68 Panali akavalo 736, abulu angʼonoangʼono 245.
O soavala’ iareoo, fiton-jato-tsi-telopolo-eneñ’ amby; o borìke vosi’eo, roanjato-tsi-efapolo-lime amby.
69 Ngamira zawo zinalipo 435 ndipo abulu analipo 6,720.
O rameva’eo, efajato-tsi-telopolo-lim’ amby naho o borìke’eo, eneñ’ arivo-tsi-fitonjato-tsi-roapolo.
70 Atsogoleri ena a mabanja anapereka mphatso zothandizira ntchito. Bwanamkubwa anapereka ku thumba losungira chuma, ndalama zagolide za makilogalamu asanu ndi atatu, mabeseni makumi asanu ndi zovala za ansembe 530.
Le amo talèn-droae’eo ty nanolotse amy fitoloñañey: i Tirsatà nanolotse bogady volamena arivo naho koveta limampolo vaho sarom-pisoroñe liman-jato-tsi-telopolo;
71 Atsogoleri ena amabanja anapereka ku thumba losungira chuma ndalama zagolide zokwana makilogalamu 168, ndiponso ndalama za siliva zokwana makilogalamu 1,250.
o talèn-droae’eo nanolotse bogady volamena ro’ale naho tsanganolo volafoty ro’arivo-tsi-roanjato amy fañajan-drala’ i fitoloñañeiy;
72 Anthu ena onse otsala anapereka ndalama zagolide zokwana makilogalamu 168, ndalama za siliva zokwana makilogalamu 140, ndiponso zovala za ansembe 67.
le natolo’ ondaty ila’eo ty bogady volamena ro’ale naho tsanganolo ro’arivo vaho sarom-pisoroñe enempolo-fito’ amby.
73 Choncho ansembe, Alevi, alonda a Nyumba ya Mulungu, anthu oyimba nyimbo, ena mwa anthu wamba, ogwira ntchito ku Nyumba ya Mulungu pamodzi ndi Aisraeli ena onse ankakhala mʼmizinda yawo. Pofika mwezi wachisanu ndi chiwiri Aisraeli onse anali atakhazikika mʼmizinda yawo.
Aa le songa nimoneñe an-drova’e ao o mpisoroñeo naho o nte-Levio naho o mpañambeñeo naho o mpisaboo naho ondaty ila’eo naho o mpitoroñ’ anjombao vaho o nte-Israele iabio, sindre tan-drova’e ao te tsatoke i volam-pahafitoy.