< Nehemiya 7 >

1 Khoma linamangidwa ndipo zitseko zinayikidwa. Pambuyo pake alonda a Nyumba ya Mulungu, oyimba nyimbo ndiponso Alevi anasankhidwa.
Postquam autem aedificatus est murus, et posui valvas, et recensui ianitores, et cantores, et Levitas:
2 Kenaka ine ndinasankha mʼbale wanga Hanani pamodzi ndi Hananiya woyangʼanira nsanja yankhondo kukhala olamulira Yerusalemu chifukwa iyeyu anali munthu odalirika ndi woopa Mulungu kuposa anthu ena.
praecepi Hanani fratri meo, et Hananiae principi domus de Ierusalem (ipse enim quasi vir verax et timens Deum plus ceteris videbatur)
3 Ine ndinawawuza kuti, “Musalole kuti zipata za Yerusalemu zitsekulidwe mpaka dzuwa litatentha, ndipo alonda asanaweruke aonetsetse kuti atseka zitseko ndi kuzipiringidza. Musankhe alonda pakati pa anthu okhala mu Yerusalemu, ena akhale pa malo pawo ndi ena akhale moyangʼanana ndi nyumba zawo.”
et dixi eis: Non aperiantur portae Ierusalem usque ad calorem solis. Cumque adhuc assisterent, clausae portae sunt, et oppilatae: et posui custodes de habitatoribus Ierusalem, singulos per vices suas, et unumquemque contra domum suam.
4 Tsono mzinda wa Yerusalemu unali wotambasuka ndiponso waukulu koma munali anthu ochepa ndipo nyumba zinali zisanamangidwe.
Civitas autem erat lata nimis et grandis, et populus parvus in medio eius, et non erant domus aedificatae.
5 Ndipo Mulungu wanga anayika mu mtima mwanga maganizo oti ndisonkhanitse anthu olemekezeka, akuluakulu ndi anthu onse kuti alembetse mayina mwa mabanja awo. Ndinapeza buku limene munalembedwa mayina a mabanja a iwo amene anayamba kubwera kuchokera ku ukapolo. Izi ndi zimene ndinazipeza zitalembedwa mʼmenemo:
Deus autem dedit in corde meo, et congregavi optimates, et magistratus, et vulgus, ut recenserem eos: et inveni librum census eorum, qui ascenderant primum, et inventum est scriptum in eo.
6 Awa ndi anthu a mʼchigawo cha Yuda amene anabwerera kuchokera ku ukapolo amene Nebukadinezara mfumu ya Babuloni anawatenga ukapolo. Iwo anabwerera ku Yerusalemu ndi ku Yuda, aliyense ku mzinda wa makolo ake.
Isti filii provinciae, qui ascenderunt de captivitate migrantium, quos transtulerat Nabuchodonosor rex Babylonis, et reversi sunt in Ierusalem, et in Iudaeam, unusquisque in civitatem suam.
7 Anabwera pamodzi ndi atsogoleri awa: Zerubabeli, Yesuwa, Nehemiya, Azariya, Raamiya, Nahamani, Mordekai, Bilisani, Misipereti, Bigivai, Nehumu ndi Baana. Tsono chiwerengero cha anthu a ku Israeli chinali chotere:
Qui venerunt cum Zorobabel, Iosue, Nehemias, Azarias, Raamias, Nahamani, Mardochaeus, Belsam, Mespharath, Begoai, Nahum, Baana. Numerus virorum populi Israel:
8 Zidzukulu za Parosi 2,172
Filii Pharos, duo millia centum septuaginta duo:
9 Zidzukulu za Sefatiya 372
Filii Saphatia, trecenti septuaginta duo:
10 Zidzukulu za Ara 652
Filii Area, sexcenti quinquaginta duo:
11 Zidzukulu za Pahati-Mowabu (kudzera mu mʼbado wa Yesuwa ndi Yowabu) 2,818
Filii Phahathmoab filiorum Iosue et Ioab, duo millia octingenti decem et octo:
12 Zidzukulu za Elamu 1,254
Filii Aelam, mille octigenti quinquagintaquattuor:
13 Zidzukulu za Zatu 845
Filii Zethua, octingenti quadragintaquinque:
14 Zidzukulu za Zakai 760
Filii Zachai, septingenti sexaginta:
15 Zidzukulu za Binuyi 648
Filii Bannui, sexcenti quadragintaocto:
16 Zidzukulu za Bebai 628
Filii Bebai, sexcenti vigintiocto:
17 Zidzukulu za Azigadi 2,322
Filii Azgad, duo millia trecenti vigintiduo:
18 Zidzukulu za Adonikamu 667
Filii Adonicam, sexcenti sexagintaseptem:
19 Zidzukulu za Abigivai 2,067
Filii Beguai, duo millia sexagintaseptem:
20 Zidzukulu za Adini 655
Filii Adin, sexcenti quinquagintaquinque:
21 Zidzukulu za Ateri (kudzera mwa Hezekiya) 98
Filii Ater, filii Hezeciae, nonagintaocto:
22 Zidzukulu za Hasumu 328
Filii Hasem, trecenti vigintiocto:
23 Zidzukulu za Bezayi 324
Filii Besai, trecenti vigintiquattuor:
24 Zidzukulu za Harifu 112
Filii Hareph, centum duodecim:
25 Zidzukulu za Gibiyoni 95.
Filii Gabaon, nonagintaquinque:
26 Anthu a ku Betelehemu ndi Netofa 188
Filii Bethlehem, et Netupha, centum octogintaocto.
27 Anthu a ku Anatoti 128
Viri Anathoth, centum vigintiocto.
28 Anthu a ku Beti-Azimaveti 42
Viri Bethazmoth, quadragintaduo.
29 Anthu a ku Kiriati Yeyarimu Kefira ndi Beeroti 743
Viri Cariathiarim, Cephira, et Beroth, septingenti quadragintatres.
30 Anthu a ku Rama ndi Geba 621
Viri Rama et Geba, sexcenti vigintiunus.
31 Anthu a ku Mikimasi 122
Viri Machmas, centum vigintiduo.
32 Anthu a ku Beteli ndi Ai 123
Viri Bethel et Hai, centum vigintitres.
33 Anthu a ku Nebo winayo 52
Viri Nebo alterius, quinquagintaduo.
34 Ana a Elamu wina 1,254
Viri Aelam alterius, mille ducenti quinquagintaquattuor.
35 Zidzukulu za Harimu 320
Filii Harem, trecenti viginti.
36 Zidzukulu za Yeriko 345
Filii Iericho, trecenti quadragintaquinque.
37 Zidzukulu za Lodi, Hadidi ndi Ono 721
Filii Lod Hadid et Ono, septingenti vigintiunus.
38 Zidzukulu za Senaya 3,930.
Filii Senaa, tria millia nongenti triginta.
39 Ansembe anali awa: A banja la Yedaya (ndiye kuti zidzukulu za Yesuwa) 973
Sacerdotes: Filii Idaia in domo Iosue, nongenti septuagintatres.
40 Zidzukulu za Imeri 1,052
Filii Emmer, mille quinquagintaduo.
41 Zidzukulu za Pasi-Huri 1,247
Filii Phashur, mille ducenti quadragintaseptem.
42 Zidzukulu za Harimu 1,017.
Filii Arem, mille decem et septem. Levitae:
43 Alevi anali awa: A banja la Yesuwa ndi Kadimieli, ndiye kuti zidzukulu za Hodaviya 74.
Filii Iosue et Cedmihel filiorum
44 Anthu oyimba: Zidzukulu za Asafu 148.
Oduiae, septuagintaquattuor. Cantores:
45 Alonda a ku Nyumba ya Mulungu anali awa: Zidzukulu za Salumu, Ateri, Talimoni, Hatita ndi Sobai 138.
Filii Asaph, centum quadragintaocto.
46 Anthu ogwira ntchito ku Nyumba ya Mulungu anali awa: Zidzukulu za Ziha, zidzukulu za Hasufa, zidzukulu za Tabaoti,
Ianitores: filii Sellum, filii Ater, filii Telmon, filii Accub, filii Hatita, filii Sobai: centum trigintaocto.
47 Zidzukulu Kerosi, zidzukulu za Siya, zidzukulu za Padoni
Nathinaei: filii Soha, filii Hasupha, filii Tebbaoth,
48 Zidzukulu za Lebana za Hagaba, ndi za Salimayi,
filii Ceros, filii Siaa, filii Phadon, filii Lebana, filii Hagaba, filii Selmai,
49 Zidzukulu za Hanani, zidzukulu za Gideli, zidzukulu za Gahari,
filii Hanan, filii Geddel, filii Gaher,
50 Zidzukulu za Reyaya, zidzukulu za Rezini, zidzukulu za Nehoda,
filii Raaia, filii Rasin, filii Necoda,
51 Zidzukulu za Gazamu, zidzukulu za Uza, zidzukulu za Paseya,
filii Gezem, filii Aza, filii Phasea,
52 Zidzukulu za Besai, zidzukulu za Meunimu, zidzukulu za Nefusimu,
filii Besai, filii Munim, filii Nephussim,
53 Zidzukulu za Bakibuku, zidzukulu za Hakufa, zidzukulu za Harihuri,
filii Bacbuc, filii Hacupha, filii Harhur,
54 Zidzukulu za Baziliti, zidzukulu za Mehida, zidzukulu za Harisa,
filii Besloth, filii Mahida, filii Harsa,
55 Zidzukulu za Barikosi, zidzukulu za Sisera, zidzukulu za Tema
filii Bercos, filii Sisara, filii Thema,
56 Zidzukulu za Neziya, ndi zidzukulu za Hatifa.
filii Nasia, filii Hatipha,
57 Zidzukulu za antchito a Solomoni: Zidzukulu za Sotai, zidzukulu za Sofereti, zidzukulu za Perida
filii servorum Salomonis, filii Sothai, filii Sophereth, filii Pharida,
58 zidzukulu za Yaala, zidzukulu za Darikoni, zidzukulu za Gideli,
filii Iahala, filii Darcon, filii Ieddel,
59 zidzukulu za Sefatiya, zidzukulu za Hatilu zidzukulu za Pokereti-Hazebaimu ndi zidzukulu Amoni.
filii Saphatia, filii Hatil, filii Phochereth, qui erat ortus ex Sabaim, filio Amon.
60 Anthu onse ogwira ntchito ku Nyumba ya Mulungu pamodzi ndi zidzukulu za antchito a Solomoni analipo 392.
Omnes Nathinaei, et filii servorum Salomonis, trecenti nonagintaduo.
61 Ali munsiwa anachokera ku Teli-Mela, Teri-Harisa, Kerubi, Adoni, ndi Imeri, koma sanathe kunena mwa tchutchutchu kuti makolo awo kapena mafuko awo analidi Aisraeli kapena ayi.
Hi sunt autem, qui ascenderunt de Thelmela, Thelharsa, Cherub, Addon, et Emmer: et non potuerunt indicare domum patrum suorum, et semen suum, utrum ex Israel essent.
62 Zidzukulu za Delaya, zidzukulu za Tobiya ndi zidzukulu za Nekoda 642.
Filii Dalaia, filii Tobia, filii Necoda, sexcenti quadragintaduo.
63 Ndiponso ena pakati pa ansembe anali awa: zidzukulu za Hobiya, zidzukulu za Hakozi ndi zidzukulu za Barizilai (munthu amene anakwatira mwana wamkazi wa Barizilai wa ku Giliyadi ndipo amatchedwa dzina limenelo).
Et de Sacerdotibus, filii Habia, filii Accos, filii Berzellai, qui accepit de filiabus Berzellai Galaaditis uxorem: et vocatus est nomine eorum.
64 Iwowa anafufuzafufuza mayina awo mʼbuku la mibado ya mabanja awo ndipo sanapeze mayina awo kotero anachotsedwa pa unsembe nawerengedwa ngati odetsedwa pa chipembedzo.
Hi quaesierunt scripturam suam in censu, et non invenerunt: et eiecti sunt de sacerdotio.
65 Choncho bwanamkubwa anawawuza anthuwo kuti asamadye nawo chakudya china chilichonse choperekedwa kwa Mulungu mpaka patapezeka wansembe wodziwa kugwiritsa bwino ntchito ya Urimu ndi Tumimu.
Dixitque Athersatha eis ut non manducarent de Sanctis sanctorum, donec staret Sacerdos doctus et eruditus.
66 Chiwerengero chonse cha anthuwa chinali 42,360.
Omnis multitudo quasi vir unus quadragintaduo millia sexcenti sexaginta,
67 Kuwonjezera pamenepa panali antchito awo aamuna ndi aakazi 7,337 ndiponso anthu aamuna ndi aakazi oyimba nyimbo okwanira 245.
absque servis et ancillis eorum, qui erant septem millia trecenti trigintaseptem, et inter eos cantores, et cantatrices, ducenti quadragintaquinque.
68 Panali akavalo 736, abulu angʼonoangʼono 245.
Equi eorum, septingenti trigintasex: muli eorum, ducenti quadragintaquinque:
69 Ngamira zawo zinalipo 435 ndipo abulu analipo 6,720.
cameli eorum, quadringenti trigintaquinque: asini, sex millia septingenti viginti.
70 Atsogoleri ena a mabanja anapereka mphatso zothandizira ntchito. Bwanamkubwa anapereka ku thumba losungira chuma, ndalama zagolide za makilogalamu asanu ndi atatu, mabeseni makumi asanu ndi zovala za ansembe 530.
Nonnulli autem de principibus familiarum dederunt in opus. Athersatha dedit in thesaurum auri drachmas mille, phialas quinquaginta, tunicas sacerdotales quingentas triginta.
71 Atsogoleri ena amabanja anapereka ku thumba losungira chuma ndalama zagolide zokwana makilogalamu 168, ndiponso ndalama za siliva zokwana makilogalamu 1,250.
Et de principibus familiarum dederunt in thesaurum operis auri drachmas viginti millia, et argenti mnas duo millia ducentas.
72 Anthu ena onse otsala anapereka ndalama zagolide zokwana makilogalamu 168, ndalama za siliva zokwana makilogalamu 140, ndiponso zovala za ansembe 67.
Et quod dedit reliquus populus, auri drachmas viginti millia, et argenti mnas duo millia, et tunicas sacerdotales sexagintaseptem.
73 Choncho ansembe, Alevi, alonda a Nyumba ya Mulungu, anthu oyimba nyimbo, ena mwa anthu wamba, ogwira ntchito ku Nyumba ya Mulungu pamodzi ndi Aisraeli ena onse ankakhala mʼmizinda yawo. Pofika mwezi wachisanu ndi chiwiri Aisraeli onse anali atakhazikika mʼmizinda yawo.
Habitaverunt autem Sacerdotes, et Levitae, et ianitores, et cantores, et reliquum vulgus, et Nathinaei, et omnis Israel in civitatibus suis.

< Nehemiya 7 >