< Nehemiya 7 >
1 Khoma linamangidwa ndipo zitseko zinayikidwa. Pambuyo pake alonda a Nyumba ya Mulungu, oyimba nyimbo ndiponso Alevi anasankhidwa.
城壁が築かれて、とびらを設け、さらに門衛、歌うたう者およびレビびとを任命したので、
2 Kenaka ine ndinasankha mʼbale wanga Hanani pamodzi ndi Hananiya woyangʼanira nsanja yankhondo kukhala olamulira Yerusalemu chifukwa iyeyu anali munthu odalirika ndi woopa Mulungu kuposa anthu ena.
わたしは、わたしの兄弟ハナニと、城のつかさハナニヤに命じて、エルサレムを治めさせた。彼は多くの者にまさって忠信な、神を恐れる者であったからである。
3 Ine ndinawawuza kuti, “Musalole kuti zipata za Yerusalemu zitsekulidwe mpaka dzuwa litatentha, ndipo alonda asanaweruke aonetsetse kuti atseka zitseko ndi kuzipiringidza. Musankhe alonda pakati pa anthu okhala mu Yerusalemu, ena akhale pa malo pawo ndi ena akhale moyangʼanana ndi nyumba zawo.”
わたしは彼らに言った、「日の暑くなるまではエルサレムのもろもろの門を開いてはならない。人々が立って守っている間に門を閉じさせ、貫の木を差せ。またエルサレムの住民の中から番兵を立てて、おのおのにその所を守らせ、またおのおのの家と向かい合う所を守らせよ」。
4 Tsono mzinda wa Yerusalemu unali wotambasuka ndiponso waukulu koma munali anthu ochepa ndipo nyumba zinali zisanamangidwe.
町は広くて大きかったが、その内の民は少なく、家々はまだ建てられていなかった。
5 Ndipo Mulungu wanga anayika mu mtima mwanga maganizo oti ndisonkhanitse anthu olemekezeka, akuluakulu ndi anthu onse kuti alembetse mayina mwa mabanja awo. Ndinapeza buku limene munalembedwa mayina a mabanja a iwo amene anayamba kubwera kuchokera ku ukapolo. Izi ndi zimene ndinazipeza zitalembedwa mʼmenemo:
時に神はわたしの心に、尊い人々、つかさおよび民を集めて、家系によってその名簿をしらべようとの思いを起された。わたしは最初に上って来た人々の系図を発見し、その中にこのようにしるしてあるのを見いだした。
6 Awa ndi anthu a mʼchigawo cha Yuda amene anabwerera kuchokera ku ukapolo amene Nebukadinezara mfumu ya Babuloni anawatenga ukapolo. Iwo anabwerera ku Yerusalemu ndi ku Yuda, aliyense ku mzinda wa makolo ake.
バビロンの王ネブカデネザルが捕え移した捕囚のうち、ゆるされてエルサレムおよびユダに上り、おのおの自分の町に帰ったこの州の人々は次のとおりである。
7 Anabwera pamodzi ndi atsogoleri awa: Zerubabeli, Yesuwa, Nehemiya, Azariya, Raamiya, Nahamani, Mordekai, Bilisani, Misipereti, Bigivai, Nehumu ndi Baana. Tsono chiwerengero cha anthu a ku Israeli chinali chotere:
彼らはゼルバベル、エシュア、ネヘミヤ、アザリヤ、ラアミヤ、ナハマニ、モルデカイ、ビルシャン、ミスペレテ、ビグワイ、ネホム、バアナと一緒に帰ってきた者たちである。そのイスラエルの民の人数は次のとおりである。
8 Zidzukulu za Parosi 2,172
パロシの子孫は二千百七十二人。
9 Zidzukulu za Sefatiya 372
シパテヤの子孫は三百七十二人。
11 Zidzukulu za Pahati-Mowabu (kudzera mu mʼbado wa Yesuwa ndi Yowabu) 2,818
パハテ・モアブの子孫すなわちエシュアとヨアブの子孫は二千八百十八人。
12 Zidzukulu za Elamu 1,254
エラムの子孫は一千二百五十四人。
14 Zidzukulu za Zakai 760
ザッカイの子孫は七百六十人。
15 Zidzukulu za Binuyi 648
ビンヌイの子孫は六百四十八人。
16 Zidzukulu za Bebai 628
ベバイの子孫は六百二十八人。
17 Zidzukulu za Azigadi 2,322
アズガデの子孫は二千三百二十二人。
18 Zidzukulu za Adonikamu 667
アドニカムの子孫は六百六十七人。
19 Zidzukulu za Abigivai 2,067
ビグワイの子孫は二千六十七人。
20 Zidzukulu za Adini 655
アデンの子孫は六百五十五人。
21 Zidzukulu za Ateri (kudzera mwa Hezekiya) 98
ヒゼキヤの家のアテルの子孫は九十八人。
22 Zidzukulu za Hasumu 328
ハシュムの子孫は三百二十八人。
23 Zidzukulu za Bezayi 324
ベザイの子孫は三百二十四人。
24 Zidzukulu za Harifu 112
ハリフの子孫は百十二人。
25 Zidzukulu za Gibiyoni 95.
ギベオンの子孫は九十五人。
26 Anthu a ku Betelehemu ndi Netofa 188
ベツレヘムおよびネトパの人々は百八十八人。
27 Anthu a ku Anatoti 128
アナトテの人々は百二十八人。
28 Anthu a ku Beti-Azimaveti 42
ベテ・アズマウテの人々は四十二人。
29 Anthu a ku Kiriati Yeyarimu Kefira ndi Beeroti 743
キリアテ・ヤリム、ケピラおよびベエロテの人々は七百四十三人。
30 Anthu a ku Rama ndi Geba 621
ラマおよびゲバの人々は六百二十一人。
31 Anthu a ku Mikimasi 122
ミクマシの人々は百二十二人。
32 Anthu a ku Beteli ndi Ai 123
ベテルおよびアイの人々は百二十三人。
33 Anthu a ku Nebo winayo 52
ほかのネボの人々は五十二人。
34 Ana a Elamu wina 1,254
ほかのエラムの子孫は一千二百五十四人。
35 Zidzukulu za Harimu 320
ハリムの子孫は三百二十人。
36 Zidzukulu za Yeriko 345
エリコの人々は三百四十五人。
37 Zidzukulu za Lodi, Hadidi ndi Ono 721
ロド、ハデデおよびオノの人々は七百二十一人。
38 Zidzukulu za Senaya 3,930.
セナアの子孫は三千九百三十人。
39 Ansembe anali awa: A banja la Yedaya (ndiye kuti zidzukulu za Yesuwa) 973
祭司では、エシュアの家のエダヤの子孫が九百七十三人。
40 Zidzukulu za Imeri 1,052
インメルの子孫が一千五十二人。
41 Zidzukulu za Pasi-Huri 1,247
パシュルの子孫が一千二百四十七人。
42 Zidzukulu za Harimu 1,017.
ハリムの子孫が一千十七人。
43 Alevi anali awa: A banja la Yesuwa ndi Kadimieli, ndiye kuti zidzukulu za Hodaviya 74.
レビびとでは、エシュアの子孫すなわちホデワの子孫のうちのカデミエルの子孫が七十四人。
44 Anthu oyimba: Zidzukulu za Asafu 148.
歌うたう者では、アサフの子孫が百四十八人。
45 Alonda a ku Nyumba ya Mulungu anali awa: Zidzukulu za Salumu, Ateri, Talimoni, Hatita ndi Sobai 138.
門衛では、シャルムの子孫、アテルの子孫、タルモンの子孫、アックブの子孫、ハテタの子孫およびショバイの子孫合わせて百三十八人。
46 Anthu ogwira ntchito ku Nyumba ya Mulungu anali awa: Zidzukulu za Ziha, zidzukulu za Hasufa, zidzukulu za Tabaoti,
宮に仕えるしもべでは、ジハの子孫、ハスパの子孫、タバオテの子孫、
47 Zidzukulu Kerosi, zidzukulu za Siya, zidzukulu za Padoni
ケロスの子孫、シアの子孫、パドンの子孫、
48 Zidzukulu za Lebana za Hagaba, ndi za Salimayi,
レバナの子孫、ハガバの子孫、サルマイの子孫、
49 Zidzukulu za Hanani, zidzukulu za Gideli, zidzukulu za Gahari,
ハナンの子孫、ギデルの子孫、ガハルの子孫、
50 Zidzukulu za Reyaya, zidzukulu za Rezini, zidzukulu za Nehoda,
レアヤの子孫、レヂンの子孫、ネコダの子孫、
51 Zidzukulu za Gazamu, zidzukulu za Uza, zidzukulu za Paseya,
ガザムの子孫、ウザの子孫、パセアの子孫、
52 Zidzukulu za Besai, zidzukulu za Meunimu, zidzukulu za Nefusimu,
ベサイの子孫、メウニムの子孫、ネフセシムの子孫、
53 Zidzukulu za Bakibuku, zidzukulu za Hakufa, zidzukulu za Harihuri,
バクブクの子孫、ハクパの子孫、ハルホルの子孫、
54 Zidzukulu za Baziliti, zidzukulu za Mehida, zidzukulu za Harisa,
バヅリテの子孫、メヒダの子孫、ハルシャの子孫、
55 Zidzukulu za Barikosi, zidzukulu za Sisera, zidzukulu za Tema
バルコスの子孫、シセラの子孫、テマの子孫、
56 Zidzukulu za Neziya, ndi zidzukulu za Hatifa.
ネヂアの子孫およびハテパの子孫。
57 Zidzukulu za antchito a Solomoni: Zidzukulu za Sotai, zidzukulu za Sofereti, zidzukulu za Perida
ソロモンのしもべであった者たちの子孫では、ソタイの子孫、ソペレテの子孫、ペリダの子孫、
58 zidzukulu za Yaala, zidzukulu za Darikoni, zidzukulu za Gideli,
ヤアラの子孫、ダルコンの子孫、ギデルの子孫、
59 zidzukulu za Sefatiya, zidzukulu za Hatilu zidzukulu za Pokereti-Hazebaimu ndi zidzukulu Amoni.
シパテヤの子孫、ハッテルの子孫、ポケレテ・ハッゼバイムの子孫、アモンの子孫。
60 Anthu onse ogwira ntchito ku Nyumba ya Mulungu pamodzi ndi zidzukulu za antchito a Solomoni analipo 392.
宮に仕えるしもべたちとソロモンのしもべであった者たちの子孫とは合わせて三百九十二人。
61 Ali munsiwa anachokera ku Teli-Mela, Teri-Harisa, Kerubi, Adoni, ndi Imeri, koma sanathe kunena mwa tchutchutchu kuti makolo awo kapena mafuko awo analidi Aisraeli kapena ayi.
テルメラ、テルハレサ、ケルブ、アドンおよびインメルから上って来た者があったが、その氏族と、血統とを示して、イスラエルの者であることを明らかにすることができなかった。その人々は次のとおりである。
62 Zidzukulu za Delaya, zidzukulu za Tobiya ndi zidzukulu za Nekoda 642.
すなわちデラヤの子孫、トビヤの子孫、ネコダの子孫であって、合わせて六百四十二人。
63 Ndiponso ena pakati pa ansembe anali awa: zidzukulu za Hobiya, zidzukulu za Hakozi ndi zidzukulu za Barizilai (munthu amene anakwatira mwana wamkazi wa Barizilai wa ku Giliyadi ndipo amatchedwa dzina limenelo).
また祭司のうちにホバヤの子孫、ハッコヅの子孫、バルジライの子孫がある。バルジライはギレアデびとバルジライの娘たちのうちから妻をめとったので、その名で呼ばれた。
64 Iwowa anafufuzafufuza mayina awo mʼbuku la mibado ya mabanja awo ndipo sanapeze mayina awo kotero anachotsedwa pa unsembe nawerengedwa ngati odetsedwa pa chipembedzo.
これらの者はこの系図に載った者のうちに、自分の籍をたずねたが、なかったので、汚れた者として祭司の職から除かれた。
65 Choncho bwanamkubwa anawawuza anthuwo kuti asamadye nawo chakudya china chilichonse choperekedwa kwa Mulungu mpaka patapezeka wansembe wodziwa kugwiritsa bwino ntchito ya Urimu ndi Tumimu.
総督は彼らに告げて、ウリムとトンミムを帯びる祭司の起るまでは、いと聖なる物を食べてはならぬと言った。
66 Chiwerengero chonse cha anthuwa chinali 42,360.
会衆は合わせて四万二千三百六十人であった。
67 Kuwonjezera pamenepa panali antchito awo aamuna ndi aakazi 7,337 ndiponso anthu aamuna ndi aakazi oyimba nyimbo okwanira 245.
このほかに男女の奴隷が七千三百三十七人、歌うたう者が男女合わせて二百四十五人あった。
68 Panali akavalo 736, abulu angʼonoangʼono 245.
その馬は七百三十六頭、その騾馬は二百四十五頭、
69 Ngamira zawo zinalipo 435 ndipo abulu analipo 6,720.
そのらくだは四百三十五頭、そのろばは六千七百二十頭であった。
70 Atsogoleri ena a mabanja anapereka mphatso zothandizira ntchito. Bwanamkubwa anapereka ku thumba losungira chuma, ndalama zagolide za makilogalamu asanu ndi atatu, mabeseni makumi asanu ndi zovala za ansembe 530.
氏族の長のうち工事のためにささげ物をした人々があった。総督は金一千ダリク、鉢五十、祭司の衣服五百三十かさねを倉に納めた。
71 Atsogoleri ena amabanja anapereka ku thumba losungira chuma ndalama zagolide zokwana makilogalamu 168, ndiponso ndalama za siliva zokwana makilogalamu 1,250.
また氏族の長のうちのある人々は金二万ダリク、銀二千二百ミナを工事のために倉に納めた。
72 Anthu ena onse otsala anapereka ndalama zagolide zokwana makilogalamu 168, ndalama za siliva zokwana makilogalamu 140, ndiponso zovala za ansembe 67.
その他の民の納めたものは金二万ダリク、銀二千ミナ、祭司の衣服六十七かさねであった。
73 Choncho ansembe, Alevi, alonda a Nyumba ya Mulungu, anthu oyimba nyimbo, ena mwa anthu wamba, ogwira ntchito ku Nyumba ya Mulungu pamodzi ndi Aisraeli ena onse ankakhala mʼmizinda yawo. Pofika mwezi wachisanu ndi chiwiri Aisraeli onse anali atakhazikika mʼmizinda yawo.
こうして祭司、レビびと、門衛、歌うたう者、民のうちのある人々、宮に仕えるしもべたち、およびイスラエルびとは皆その町々に住んだ。イスラエルの人々はその町々に住んで七月になった。