< Nehemiya 7 >

1 Khoma linamangidwa ndipo zitseko zinayikidwa. Pambuyo pake alonda a Nyumba ya Mulungu, oyimba nyimbo ndiponso Alevi anasankhidwa.
Setelah benteng Yerusalem selesai dibangun dan pintu-pintu gerbangnya sudah dipasang, kami menunjuk sejumlah orang sebagai penjaga gerbang. Selain itu, ditetapkan juga orang-orang Lewi yang bertugas di rumah TUHAN untuk menjadi penyanyi, pemain musik, dan petugas-petugas lainnya.
2 Kenaka ine ndinasankha mʼbale wanga Hanani pamodzi ndi Hananiya woyangʼanira nsanja yankhondo kukhala olamulira Yerusalemu chifukwa iyeyu anali munthu odalirika ndi woopa Mulungu kuposa anthu ena.
Kemudian saya mengangkat dua orang untuk bertanggung jawab mengelola kota Yerusalem, yaitu Hanani saudara saya, dan Hananya, komandan benteng. Dia dapat dipercaya dan memiliki rasa hormat kepada Allah melebihi orang-orang lain.
3 Ine ndinawawuza kuti, “Musalole kuti zipata za Yerusalemu zitsekulidwe mpaka dzuwa litatentha, ndipo alonda asanaweruke aonetsetse kuti atseka zitseko ndi kuzipiringidza. Musankhe alonda pakati pa anthu okhala mu Yerusalemu, ena akhale pa malo pawo ndi ena akhale moyangʼanana ndi nyumba zawo.”
Saya memberi perintah, “Pintu gerbang Yerusalem hanya boleh dibuka ketika hari sudah siang, dan harus selalu ditutup serta dipalang ketika para penjaga masih bertugas. Tunjuklah orang-orang yang tinggal di kota Yerusalem sebagai penjaga, dan tugaskanlah beberapa dari mereka di pos-pos penjagaan dan di wilayah tempat tinggalnya masing-masing.”
4 Tsono mzinda wa Yerusalemu unali wotambasuka ndiponso waukulu koma munali anthu ochepa ndipo nyumba zinali zisanamangidwe.
Kota Yerusalem sangat luas dan lapang, tetapi penduduknya saat itu masih sedikit dan rumah-rumah di dalamnya belum dibangun kembali.
5 Ndipo Mulungu wanga anayika mu mtima mwanga maganizo oti ndisonkhanitse anthu olemekezeka, akuluakulu ndi anthu onse kuti alembetse mayina mwa mabanja awo. Ndinapeza buku limene munalembedwa mayina a mabanja a iwo amene anayamba kubwera kuchokera ku ukapolo. Izi ndi zimene ndinazipeza zitalembedwa mʼmenemo:
Lalu Allah memberi hikmat kepada saya untuk mengumpulkan para bangsawan, pemimpin, dan rakyat biasa untuk mencatat silsilah keluarga mereka masing-masing. Saya juga mendapati daftar nama dan silsilah rombongan pertama yang pulang dari pembuangan di Babel.
6 Awa ndi anthu a mʼchigawo cha Yuda amene anabwerera kuchokera ku ukapolo amene Nebukadinezara mfumu ya Babuloni anawatenga ukapolo. Iwo anabwerera ku Yerusalemu ndi ku Yuda, aliyense ku mzinda wa makolo ake.
Berikut ini adalah daftar kelompok orang yang kembali dari pembuangan, yaitu mereka yang dahulu dibawa Raja Nebukadnezar ke Babel, tetapi sekarang sudah kembali ke tempat asal mereka di Yerusalem dan di kota-kota Yehuda.
7 Anabwera pamodzi ndi atsogoleri awa: Zerubabeli, Yesuwa, Nehemiya, Azariya, Raamiya, Nahamani, Mordekai, Bilisani, Misipereti, Bigivai, Nehumu ndi Baana. Tsono chiwerengero cha anthu a ku Israeli chinali chotere:
Mereka kembali dalam satu rombongan besar bersama Zerubabel, Yesua, Nehemia, Azarya, Raamya, Nahamani, Mordekai, Bilsan, Misperet, Bigwai, Nehum, dan Baana. Berikut ini adalah daftar nama kaum keluarga bangsa Israel yang kembali, beserta jumlah rombongannya:
8 Zidzukulu za Parosi 2,172
Keturunan Paros— 2.172 orang,
9 Zidzukulu za Sefatiya 372
Keturunan Sefaca— 372 orang,
10 Zidzukulu za Ara 652
Keturunan Ara— 652 orang,
11 Zidzukulu za Pahati-Mowabu (kudzera mu mʼbado wa Yesuwa ndi Yowabu) 2,818
Keluarga Yesua dan Yoab, yang adalah anak Pahat Moab— 2.818 orang,
12 Zidzukulu za Elamu 1,254
Keturunan Elam— 1.254 orang,
13 Zidzukulu za Zatu 845
Keturunan Zatu— 845 orang,
14 Zidzukulu za Zakai 760
Keturunan Zakai— 760 orang,
15 Zidzukulu za Binuyi 648
Keturunan Binui— 648 orang,
16 Zidzukulu za Bebai 628
Keturunan Bebai— 628 orang,
17 Zidzukulu za Azigadi 2,322
Keturunan Azgad— 2.322 orang,
18 Zidzukulu za Adonikamu 667
Keturunan Adonikam— 667 orang,
19 Zidzukulu za Abigivai 2,067
Keturunan Bigwai— 2.067 orang,
20 Zidzukulu za Adini 655
Keturunan Adin— 655 orang,
21 Zidzukulu za Ateri (kudzera mwa Hezekiya) 98
Keluarga Hiskia, yaitu keturunan Ater— 98 orang,
22 Zidzukulu za Hasumu 328
Keturunan Hasum— 328 orang,
23 Zidzukulu za Bezayi 324
Keturunan Besai— 324 orang,
24 Zidzukulu za Harifu 112
Keturunan Harif— 112 orang,
25 Zidzukulu za Gibiyoni 95.
Keturunan Gibeon— 95 orang.
26 Anthu a ku Betelehemu ndi Netofa 188
Berikut ini adalah jumlah orang yang kembali, dihitung berdasarkan kota asal mereka: Betlehem dan Netofa— 188 orang,
27 Anthu a ku Anatoti 128
Anatot— 128 orang,
28 Anthu a ku Beti-Azimaveti 42
Bet Azmawet— 42 orang,
29 Anthu a ku Kiriati Yeyarimu Kefira ndi Beeroti 743
Kiryat Yearim, Kefira, dan Beerot— 743 orang,
30 Anthu a ku Rama ndi Geba 621
Rama dan Geba— 621 orang,
31 Anthu a ku Mikimasi 122
Mikmas— 122 orang,
32 Anthu a ku Beteli ndi Ai 123
Betel dan Ai— 123 orang,
33 Anthu a ku Nebo winayo 52
Nebo yang lain— 52 orang,
34 Ana a Elamu wina 1,254
Elam yang lain— 1.254 orang,
35 Zidzukulu za Harimu 320
Harim— 320 orang,
36 Zidzukulu za Yeriko 345
Yeriko— 345 orang,
37 Zidzukulu za Lodi, Hadidi ndi Ono 721
Lod, Hadid, dan Ono— 721 orang,
38 Zidzukulu za Senaya 3,930.
Sena— 3.930 orang.
39 Ansembe anali awa: A banja la Yedaya (ndiye kuti zidzukulu za Yesuwa) 973
Berikut ini adalah daftar nama kaum keluarga para imam yang kembali dari pembuangan: Keluarga Yedaya, yaitu keturunan Yesua— 973 orang,
40 Zidzukulu za Imeri 1,052
Keturunan Imer— 1.052 orang,
41 Zidzukulu za Pasi-Huri 1,247
Keturunan Pasyur— 1.247 orang,
42 Zidzukulu za Harimu 1,017.
Keturunan Harim— 1.017 orang.
43 Alevi anali awa: A banja la Yesuwa ndi Kadimieli, ndiye kuti zidzukulu za Hodaviya 74.
Berikut ini adalah daftar kelompok keturunan Lewi yang kembali dari pembuangan beserta jumlah rombongannya: Keluarga Yesua dan Kadmiel, yang adalah keturunan Hodewa— 74 orang.
44 Anthu oyimba: Zidzukulu za Asafu 148.
Pemain musik di rumah TUHAN dari keturunan Asaf— 148 orang.
45 Alonda a ku Nyumba ya Mulungu anali awa: Zidzukulu za Salumu, Ateri, Talimoni, Hatita ndi Sobai 138.
Penjaga gerbang rumah TUHAN keturunan Salum, Ater, Talmon, Akub, Hatita, dan Sobai— 138 orang.
46 Anthu ogwira ntchito ku Nyumba ya Mulungu anali awa: Zidzukulu za Ziha, zidzukulu za Hasufa, zidzukulu za Tabaoti,
Berikut ini adalah daftar nama kaum keluarga para pekerja di rumah TUHAN yang kembali dari pembuangan: Ziha, Hasufa, Tabaot,
47 Zidzukulu Kerosi, zidzukulu za Siya, zidzukulu za Padoni
Keros, Sia, Padon,
48 Zidzukulu za Lebana za Hagaba, ndi za Salimayi,
Lebana, Hagaba, Salmai,
49 Zidzukulu za Hanani, zidzukulu za Gideli, zidzukulu za Gahari,
Hanan, Gidel, Gahar,
50 Zidzukulu za Reyaya, zidzukulu za Rezini, zidzukulu za Nehoda,
Reaya, Rezin, Nekoda,
51 Zidzukulu za Gazamu, zidzukulu za Uza, zidzukulu za Paseya,
Gazam, Uza, Paseah,
52 Zidzukulu za Besai, zidzukulu za Meunimu, zidzukulu za Nefusimu,
Besai, Meunim, Nefusim,
53 Zidzukulu za Bakibuku, zidzukulu za Hakufa, zidzukulu za Harihuri,
Bakbuk, Hakufa, Harhur,
54 Zidzukulu za Baziliti, zidzukulu za Mehida, zidzukulu za Harisa,
Bazlut, Mehida, Harsa,
55 Zidzukulu za Barikosi, zidzukulu za Sisera, zidzukulu za Tema
Barkos, Sisera, Temah,
56 Zidzukulu za Neziya, ndi zidzukulu za Hatifa.
Neziah, dan Hatifa.
57 Zidzukulu za antchito a Solomoni: Zidzukulu za Sotai, zidzukulu za Sofereti, zidzukulu za Perida
Berikut ini adalah daftar nama kaum keluarga pelayan Raja Salomo yang kembali dari pembuangan: Sotai, Soferet, Perida,
58 zidzukulu za Yaala, zidzukulu za Darikoni, zidzukulu za Gideli,
Yaala, Darkon, Gidel,
59 zidzukulu za Sefatiya, zidzukulu za Hatilu zidzukulu za Pokereti-Hazebaimu ndi zidzukulu Amoni.
Sefaca, Hatil, Pokeret Hazebarim, dan Amon.
60 Anthu onse ogwira ntchito ku Nyumba ya Mulungu pamodzi ndi zidzukulu za antchito a Solomoni analipo 392.
Jumlah seluruh keturunan para pekerja rumah TUHAN dan pelayan Raja Salomo adalah 392 orang.
61 Ali munsiwa anachokera ku Teli-Mela, Teri-Harisa, Kerubi, Adoni, ndi Imeri, koma sanathe kunena mwa tchutchutchu kuti makolo awo kapena mafuko awo analidi Aisraeli kapena ayi.
Ada juga rombongan lain sejumlah 642 orang yang kembali ke Yerusalem dari kota-kota di Persia, yaitu kota Tel Melah, Tel Harsa, Kerub, Adon, dan Imer. Mereka mengaku berasal dari kaum keluarga Delaya, Tobia, dan Nekoda. Namun, mereka tidak memiliki daftar silsilah keluarga sehingga tidak ada bukti bahwa mereka keturunan Israel.
62 Zidzukulu za Delaya, zidzukulu za Tobiya ndi zidzukulu za Nekoda 642.
63 Ndiponso ena pakati pa ansembe anali awa: zidzukulu za Hobiya, zidzukulu za Hakozi ndi zidzukulu za Barizilai (munthu amene anakwatira mwana wamkazi wa Barizilai wa ku Giliyadi ndipo amatchedwa dzina limenelo).
Para imam dari kaum keluarga Hobaya, Hakos, dan Barzilai juga kembali ke Yerusalem. Ketiga kaum tersebut tidak dapat membuktikan silsilah keluarga mereka sehingga tidak boleh melayani sebagai imam. (Barzilai mendapatkan namanya itu sesuai nama ayah mertuanya, karena dia menikah dengan anak perempuan orang Gilead yang bernama Barzilai.)
64 Iwowa anafufuzafufuza mayina awo mʼbuku la mibado ya mabanja awo ndipo sanapeze mayina awo kotero anachotsedwa pa unsembe nawerengedwa ngati odetsedwa pa chipembedzo.
65 Choncho bwanamkubwa anawawuza anthuwo kuti asamadye nawo chakudya china chilichonse choperekedwa kwa Mulungu mpaka patapezeka wansembe wodziwa kugwiritsa bwino ntchito ya Urimu ndi Tumimu.
Gubernur Yehuda melarang mereka memakan makanan yang sudah dipersembahkan kepada Allah sebelum ada seorang imam yang dapat menyelesaikan masalah ini dengan meminta petunjuk Allah dengan menggunakan Urim dan Tumim.
66 Chiwerengero chonse cha anthuwa chinali 42,360.
Jumlah semua orang yang kembali ke Yehuda dari pembuangan di Persia adalah 42.360 orang.
67 Kuwonjezera pamenepa panali antchito awo aamuna ndi aakazi 7,337 ndiponso anthu aamuna ndi aakazi oyimba nyimbo okwanira 245.
Selain itu ada 7.337 orang budak, baik laki-laki maupun perempuan. Budak yang bertugas sebagai penyanyi berjumlah 245 orang, baik laki-laki maupun perempuan.
68 Panali akavalo 736, abulu angʼonoangʼono 245.
Berikut ini jumlah hewan peliharaan yang dibawa kembali oleh seluruh orang Israel: kuda— 736 ekor, bagal— 245 ekor,
69 Ngamira zawo zinalipo 435 ndipo abulu analipo 6,720.
unta— 435 ekor, keledai— 6.720 ekor.
70 Atsogoleri ena a mabanja anapereka mphatso zothandizira ntchito. Bwanamkubwa anapereka ku thumba losungira chuma, ndalama zagolide za makilogalamu asanu ndi atatu, mabeseni makumi asanu ndi zovala za ansembe 530.
Berikut ini adalah daftar sumbangan untuk biaya pembangunan kembali rumah TUHAN: Dari gubernur— 8,5 kilogram emas, 50 mangkok untuk digunakan di rumah TUHAN, dan 530 jubah untuk para imam.
71 Atsogoleri ena amabanja anapereka ku thumba losungira chuma ndalama zagolide zokwana makilogalamu 168, ndiponso ndalama za siliva zokwana makilogalamu 1,250.
Dari sejumlah kepala kaum keluarga— 170 kilogram emas, 1.200 kilogram perak.
72 Anthu ena onse otsala anapereka ndalama zagolide zokwana makilogalamu 168, ndalama za siliva zokwana makilogalamu 140, ndiponso zovala za ansembe 67.
Dari rakyat— 170 kilogram emas dan 67 jubah untuk para imam.
73 Choncho ansembe, Alevi, alonda a Nyumba ya Mulungu, anthu oyimba nyimbo, ena mwa anthu wamba, ogwira ntchito ku Nyumba ya Mulungu pamodzi ndi Aisraeli ena onse ankakhala mʼmizinda yawo. Pofika mwezi wachisanu ndi chiwiri Aisraeli onse anali atakhazikika mʼmizinda yawo.
Jadi, seluruh kelompok tersebut, yakni para imam, orang suku Lewi, penjaga gerbang rumah TUHAN, pemusik, pekerja di rumah TUHAN, dan rakyat Israel yang lain kembali ke kota-kota asal mereka. Pada bulan ketujuh, mereka sudah menetap di kotanya masing-masing.

< Nehemiya 7 >