< Nehemiya 7 >
1 Khoma linamangidwa ndipo zitseko zinayikidwa. Pambuyo pake alonda a Nyumba ya Mulungu, oyimba nyimbo ndiponso Alevi anasankhidwa.
Or, après que la muraille fut rebâtie, et que j'eus mis les portes, et qu'on eut fait une revue des chantres et des Lévites;
2 Kenaka ine ndinasankha mʼbale wanga Hanani pamodzi ndi Hananiya woyangʼanira nsanja yankhondo kukhala olamulira Yerusalemu chifukwa iyeyu anali munthu odalirika ndi woopa Mulungu kuposa anthu ena.
Je commandai à Hanani mon frère, et à Hanania capitaine de la forteresse de Jérusalem; car il était tel qu'un homme fidèle [doit] être, et il craignait Dieu plus que plusieurs [autres];
3 Ine ndinawawuza kuti, “Musalole kuti zipata za Yerusalemu zitsekulidwe mpaka dzuwa litatentha, ndipo alonda asanaweruke aonetsetse kuti atseka zitseko ndi kuzipiringidza. Musankhe alonda pakati pa anthu okhala mu Yerusalemu, ena akhale pa malo pawo ndi ena akhale moyangʼanana ndi nyumba zawo.”
Et je leur dis: Que les portes de Jérusalem ne s'ouvrent point jusqu'à la chaleur du soleil; et quand ceux qui se tiendront [là] auront fermé les portes, examinez-[les]: et qu'on pose des gardes d'entre les habitants de Jérusalem, chacun selon sa garde, et chacun vis-à-vis de sa maison.
4 Tsono mzinda wa Yerusalemu unali wotambasuka ndiponso waukulu koma munali anthu ochepa ndipo nyumba zinali zisanamangidwe.
Or la ville était spacieuse et grande, mais il y avait peu de peuple, et ses maisons n'étaient point bâties.
5 Ndipo Mulungu wanga anayika mu mtima mwanga maganizo oti ndisonkhanitse anthu olemekezeka, akuluakulu ndi anthu onse kuti alembetse mayina mwa mabanja awo. Ndinapeza buku limene munalembedwa mayina a mabanja a iwo amene anayamba kubwera kuchokera ku ukapolo. Izi ndi zimene ndinazipeza zitalembedwa mʼmenemo:
Et mon Dieu me mit au cœur d'assembler les principaux et les magistrats, et le peuple, pour en faire le dénombrement selon leurs généalogies; et je trouvai le registre du dénombrement selon les généalogies de ceux qui étaient montés la première fois; et j'y trouvai ainsi écrit:
6 Awa ndi anthu a mʼchigawo cha Yuda amene anabwerera kuchokera ku ukapolo amene Nebukadinezara mfumu ya Babuloni anawatenga ukapolo. Iwo anabwerera ku Yerusalemu ndi ku Yuda, aliyense ku mzinda wa makolo ake.
Ce sont ici ceux de la Province qui remontèrent de la captivité, d'entre ceux qui avaient été transportés, lesquels Nébuchadnetsar Roi de Babylone avait transportés, et qui retournèrent à Jérusalem et en Judée, chacun en sa ville;
7 Anabwera pamodzi ndi atsogoleri awa: Zerubabeli, Yesuwa, Nehemiya, Azariya, Raamiya, Nahamani, Mordekai, Bilisani, Misipereti, Bigivai, Nehumu ndi Baana. Tsono chiwerengero cha anthu a ku Israeli chinali chotere:
Qui vinrent avec Zorobabel, Jésuah, Néhémie, Hazaria, Rahamia, Nahamani, Mardochée, Bisan, Mitspéreth, Begvaï, Néhum, et Bahana; le nombre, [dis-je], des hommes du peuple d'Israël [est tel.]
8 Zidzukulu za Parosi 2,172
Les enfants de Parhos, deux mille cent soixante et douze.
9 Zidzukulu za Sefatiya 372
Les enfants de Séphatia, trois cent soixante et douze.
Les enfants d'Arah, six cent cinquante-deux.
11 Zidzukulu za Pahati-Mowabu (kudzera mu mʼbado wa Yesuwa ndi Yowabu) 2,818
Les enfants de Pahath-Moab, des enfants de Jésuah et de Joab, deux mille huit cent dix-huit.
12 Zidzukulu za Elamu 1,254
Les enfants de Hélam, mille deux cent cinquante-quatre.
Les enfants de Zattu, huit cent quarante-cinq.
14 Zidzukulu za Zakai 760
Les enfants de Zaccaï, sept cent soixante.
15 Zidzukulu za Binuyi 648
Les enfants de Binnui, six cent quarante-huit.
16 Zidzukulu za Bebai 628
Les enfants de Bébaï, six cent vingt-huit.
17 Zidzukulu za Azigadi 2,322
Les enfants de Hazgad, deux mille trois cent vingt-deux.
18 Zidzukulu za Adonikamu 667
Les enfants d'Adonikam, six cent soixante-sept.
19 Zidzukulu za Abigivai 2,067
Les enfants de Bigvaï, deux mille soixante-sept.
20 Zidzukulu za Adini 655
Les enfants de Hadin, six cent cinquante-cinq.
21 Zidzukulu za Ateri (kudzera mwa Hezekiya) 98
Les enfants d'Ater, [issu] d'Ezéchias, quatre-vingt-dix-huit.
22 Zidzukulu za Hasumu 328
Les enfants de Hasum, trois cent vingt-huit.
23 Zidzukulu za Bezayi 324
Les enfants de Betsaï, trois cent vingt-quatre.
24 Zidzukulu za Harifu 112
Les enfants de Harib, cent douze.
25 Zidzukulu za Gibiyoni 95.
Les enfants de Gabaon, quatre-vingt-quinze.
26 Anthu a ku Betelehemu ndi Netofa 188
Les gens de Bethléhem et de Nétopha, cent quatre-vingt-huit.
27 Anthu a ku Anatoti 128
Les gens d'Hanathoth, cent vingt-huit.
28 Anthu a ku Beti-Azimaveti 42
Les gens de Beth-Hazmaveth, quarante-deux.
29 Anthu a ku Kiriati Yeyarimu Kefira ndi Beeroti 743
Les gens de Kiriath-Jéharim, de Képhira et de Béeroth, sept cent quarante-trois.
30 Anthu a ku Rama ndi Geba 621
Les gens de Rama et de Guébah, six cent vingt et un.
31 Anthu a ku Mikimasi 122
Les gens de Micmas, cent vingt-deux.
32 Anthu a ku Beteli ndi Ai 123
Les gens de Béthel, et de Haï, cent vingt-trois.
33 Anthu a ku Nebo winayo 52
Les gens de l'autre Nébo, cinquante-deux.
34 Ana a Elamu wina 1,254
Les enfants d'un autre Hélam, mille deux cent cinquante-quatre.
35 Zidzukulu za Harimu 320
Les enfants de Harim, trois cent vingt.
36 Zidzukulu za Yeriko 345
Les enfants de Jéricho, trois cent quarante-cinq.
37 Zidzukulu za Lodi, Hadidi ndi Ono 721
Les enfants de Lod, de Hadid et d'Ono, sept cent vingt et un.
38 Zidzukulu za Senaya 3,930.
Les enfants de Sénaa, trois mille neuf cent trente.
39 Ansembe anali awa: A banja la Yedaya (ndiye kuti zidzukulu za Yesuwa) 973
Des Sacrificateurs: Les enfants de Jédahia, de la maison de Jésuah, neuf cent soixante et treize.
40 Zidzukulu za Imeri 1,052
Les enfants d'Immer, mille cinquante-deux.
41 Zidzukulu za Pasi-Huri 1,247
Les enfants de Pashur, mille deux cent quarante-sept.
42 Zidzukulu za Harimu 1,017.
Les enfants de Harim, mille dix-sept.
43 Alevi anali awa: A banja la Yesuwa ndi Kadimieli, ndiye kuti zidzukulu za Hodaviya 74.
Des Lévites: Les enfants de Jésuah et de Kadmiel, d'entre les enfants de Hodeva, soixante quatorze.
44 Anthu oyimba: Zidzukulu za Asafu 148.
Des chantres: Les enfants d'Asaph, cent quarante-huit.
45 Alonda a ku Nyumba ya Mulungu anali awa: Zidzukulu za Salumu, Ateri, Talimoni, Hatita ndi Sobai 138.
Des portiers: Les enfants de Sallum, les enfants d'Ater, les enfants de Talmon, les enfants d'Hakkub, les enfantsde Hattita, les enfants de Sobaï, cent trente-huit.
46 Anthu ogwira ntchito ku Nyumba ya Mulungu anali awa: Zidzukulu za Ziha, zidzukulu za Hasufa, zidzukulu za Tabaoti,
Des Néthiniens: Les enfants de Tsiha, les enfants de Hasupha, les enfants de Tabbahoth,
47 Zidzukulu Kerosi, zidzukulu za Siya, zidzukulu za Padoni
Les enfants de Kéros, les enfants de Siha, les enfants de Padon,
48 Zidzukulu za Lebana za Hagaba, ndi za Salimayi,
Les enfants de Lebana, les enfants de Hagaba, les enfants de Salmaï,
49 Zidzukulu za Hanani, zidzukulu za Gideli, zidzukulu za Gahari,
Les enfants de Hanan, les enfants de Guiddel, les enfants de Gahar,
50 Zidzukulu za Reyaya, zidzukulu za Rezini, zidzukulu za Nehoda,
Les enfants de Réaja, les enfants de Retsin, les enfants de Nékoda,
51 Zidzukulu za Gazamu, zidzukulu za Uza, zidzukulu za Paseya,
Les enfants de Gazam, les enfants de Huza, les enfants de Paséah,
52 Zidzukulu za Besai, zidzukulu za Meunimu, zidzukulu za Nefusimu,
Les enfants de Bésaï, les enfants de Méhunim, les enfants de Néphisésim,
53 Zidzukulu za Bakibuku, zidzukulu za Hakufa, zidzukulu za Harihuri,
Les enfants de Bakbuk, les enfants de Hakupha, les enfants de Harhur,
54 Zidzukulu za Baziliti, zidzukulu za Mehida, zidzukulu za Harisa,
Les enfants de Batslith, les enfants de Méhida, les enfants de Harsa,
55 Zidzukulu za Barikosi, zidzukulu za Sisera, zidzukulu za Tema
Les enfants de Barkos, les enfants de Sisra, les enfants de Témah,
56 Zidzukulu za Neziya, ndi zidzukulu za Hatifa.
Les enfants de Netsiah, les enfants de Hatipha.
57 Zidzukulu za antchito a Solomoni: Zidzukulu za Sotai, zidzukulu za Sofereti, zidzukulu za Perida
Des enfants des serviteurs de Salomon: Les enfants de Sotaï, les enfants de Sophéreth, les enfants de Périda,
58 zidzukulu za Yaala, zidzukulu za Darikoni, zidzukulu za Gideli,
Les enfants de Jahala, les enfants de Darkon, les enfants de Guiddel,
59 zidzukulu za Sefatiya, zidzukulu za Hatilu zidzukulu za Pokereti-Hazebaimu ndi zidzukulu Amoni.
Les enfants de Séphatia, les enfants de Hattil, les enfants de Pockereth-Hatsébajim, les enfants d'Amon.
60 Anthu onse ogwira ntchito ku Nyumba ya Mulungu pamodzi ndi zidzukulu za antchito a Solomoni analipo 392.
Tous les Néthiniens, et les enfants des serviteurs de Salomon, étaient trois cent quatre-vingt-douze.
61 Ali munsiwa anachokera ku Teli-Mela, Teri-Harisa, Kerubi, Adoni, ndi Imeri, koma sanathe kunena mwa tchutchutchu kuti makolo awo kapena mafuko awo analidi Aisraeli kapena ayi.
Or ce sont ici ceux qui montèrent de Telmelah, de Tel-Harsa, de Kérub, d'Addon et d'Immer, lesquels ne purent montrer la maison de leurs pères, ni leur race, [pour savoir] s'ils étaient d'Israël.
62 Zidzukulu za Delaya, zidzukulu za Tobiya ndi zidzukulu za Nekoda 642.
Les enfants de Délaja, les enfants de Tobija, les enfants de Nékoda, six cent quarante-deux.
63 Ndiponso ena pakati pa ansembe anali awa: zidzukulu za Hobiya, zidzukulu za Hakozi ndi zidzukulu za Barizilai (munthu amene anakwatira mwana wamkazi wa Barizilai wa ku Giliyadi ndipo amatchedwa dzina limenelo).
Et des Sacrificateurs: Les enfants de Habaja, les enfants de Kots, les enfants de Barzillaï, qui prit pour femme une des filles de Barzillaï Galaadite, et qui fut appelé de leur nom.
64 Iwowa anafufuzafufuza mayina awo mʼbuku la mibado ya mabanja awo ndipo sanapeze mayina awo kotero anachotsedwa pa unsembe nawerengedwa ngati odetsedwa pa chipembedzo.
Ils cherchèrent leur registre en recherchant leur généalogie, mais ils n'y furent point trouvés; c'est pourquoi ils furent exclus de la Sacrificature.
65 Choncho bwanamkubwa anawawuza anthuwo kuti asamadye nawo chakudya china chilichonse choperekedwa kwa Mulungu mpaka patapezeka wansembe wodziwa kugwiritsa bwino ntchito ya Urimu ndi Tumimu.
Et Attirsatha leur dit; qu'ils ne mangeassent point des choses très-saintes, jusqu'à ce que le Sacrificateur assistât avec l'Urim et le Thummim.
66 Chiwerengero chonse cha anthuwa chinali 42,360.
Toute l'assemblée réunie était de quarante-deux mille trois cent soixante;
67 Kuwonjezera pamenepa panali antchito awo aamuna ndi aakazi 7,337 ndiponso anthu aamuna ndi aakazi oyimba nyimbo okwanira 245.
Sans leurs serviteurs et leurs servantes, qui étaient sept mille trois cent trente-sept; et ils avaient deux cent quarante-cinq chantres ou chanteuses.
68 Panali akavalo 736, abulu angʼonoangʼono 245.
Ils avaient sept cent trente-six chevaux, deux cent quarante-cinq mulets;
69 Ngamira zawo zinalipo 435 ndipo abulu analipo 6,720.
Quatre cent trente-cinq chameaux, et six mille sept cent vingt ânes.
70 Atsogoleri ena a mabanja anapereka mphatso zothandizira ntchito. Bwanamkubwa anapereka ku thumba losungira chuma, ndalama zagolide za makilogalamu asanu ndi atatu, mabeseni makumi asanu ndi zovala za ansembe 530.
Or quelques-uns des Chefs des pères contribuèrent pour l'ouvrage. Attirsatha donna au trésor mille drachmes d'or, cinquante bassins, cinq cent trente robes de Sacrificateurs.
71 Atsogoleri ena amabanja anapereka ku thumba losungira chuma ndalama zagolide zokwana makilogalamu 168, ndiponso ndalama za siliva zokwana makilogalamu 1,250.
Et quelques autres d'entre les Chefs des pères donnèrent pour le trésor de l'ouvrage, vingt mille drachmes d'or, et deux mille deux cent mines d'argent.
72 Anthu ena onse otsala anapereka ndalama zagolide zokwana makilogalamu 168, ndalama za siliva zokwana makilogalamu 140, ndiponso zovala za ansembe 67.
Et ce que le reste du peuple donna, fut vingt mille drachmes d'or, et deux mille mines d'argent, et soixante-sept robes de Sacrificateurs.
73 Choncho ansembe, Alevi, alonda a Nyumba ya Mulungu, anthu oyimba nyimbo, ena mwa anthu wamba, ogwira ntchito ku Nyumba ya Mulungu pamodzi ndi Aisraeli ena onse ankakhala mʼmizinda yawo. Pofika mwezi wachisanu ndi chiwiri Aisraeli onse anali atakhazikika mʼmizinda yawo.
Et ainsi les Sacrificateurs, les Lévites, les portiers, les chantres, quelques-uns du peuple, les Néthiniens, et tous ceux d'Israël habitèrent dans leurs villes; de sorte que quand le septième mois approcha, les enfants d'Israël étaient dans leurs villes.