< Nehemiya 4 >

1 Sanibalati atamva kuti tikumanganso khoma anapsa mtima nayamba kuseka ndi kunyogodola Ayuda kwambiri.
Кынд а аузит Санбалат кэ зидим ярэшь зидул, с-а мыният ши с-а супэрат фоарте таре. Шь-а бэтут жок де иудей
2 Ndipo anayankhula pamaso pa abale ake ndi asilikali a Samariya kuti, “Kodi Ayuda ofowokawa akuchita chiyani? Kodi iwo nʼkumanganso khoma? Kodi adzaperekanso nsembe? Kodi adzatsiriza ntchitoyi tsiku limodzi? Kodi adzachita kutenga miyala yakale ija ndi mmene inapseramo?”
ши а зис ынаинтя фрацилор сэй ши ынаинтя осташилор Самарией: „Ла че лукрязэ ачешть иудей непутинчошь? Оаре вор фи лэсаць сэ лукрезе? Оаре вор жертфи? Оаре вор испрэви? Оаре вор да ей вяцэ унор петре ынмормынтате суб мормане де праф ши арсе де фок?”
3 Tobiya wa ku Amoni, amene anali naye anati, “Chimene akumangacho ngati nkhandwe itakwerapo, itha kugwetsa khoma lawolo!”
Тобия, Амонитул, ера лынгэ ел ши а зис: „Сэ зидяскэ нумай! Дакэ се ва суи о вулпе, ле ва дэрыма зидул лор де пятрэ.”
4 Tsono ndinayamba kupemphera kuti, “Timvereni, Inu Mulungu wathu, mmene akutinyozera. Mulole kuti mawu awo onyoza awabwerere, ndipo atengedwe ukapolo ku dziko lachilendo.
„Аскултэ, Думнезеул ностру, кум сунтем батжокориць! Фэ сэ кадэ окэриле лор асупра капулуй лор ши дэ-й прадэ пе ун пэмынт унде сэ фие робь.
5 Musawakhululukire mphulupulu zawo kapena kufafaniza machimo awo pamaso panu popeza aputa ukali wanu pamaso pa anthu omanga khoma.”
Ну ле ерта фэрэделеӂя, ши пэкатул лор сэ ну фие штерс динаинтя Та, кэч ау некэжит пе чей че зидеск.”
6 Choncho ife tinamangabe khomalo kufikira lonse litafika theka la msinkhu wake, chifukwa chakuti anthu anagwira ntchitoyo ndi mtima wawo wonse.
Ам зидит зидул, каре а фост испрэвит претутиндень пынэ ла жумэтате дин ынэлцимя луй. Ши попорул лукра ку инимэ.
7 Koma pamene Sanibalati, Tobiya, Aarabu, Aamoni ndi anthu a ku Asidodi anamva kuti ntchito yokonzanso makoma a Yerusalemu ikupitirirabe ndipo kuti mipata ikutsekedwa, anapsa mtima kwambiri.
Дар Санбалат, Тобия, арабий, амониций ши асдодиций с-ау супэрат фоарте таре кынд ау аузит кэ дреӂеря зидурилор ынаинта ши кэ спэртуриле ынчепяу сэ се аступе.
8 Tsono onse anapangana za chiwembu kuti abwere ndi kudzathira nkhondo anthu a ku Yerusalemu ndi kuyambitsa mapokoso pakati pawo.
С-ау унит тоць ымпреунэ ка сэ винэ ымпотрива Иерусалимулуй ши сэ-й факэ стрикэчунь.
9 Koma ife tinapemphera kwa Mulungu wathu ndipo tinayika alonda otiteteza kwa adaniwo usiku ndi usana.
Не-ам ругат Думнезеулуй ностру ши ам пус о стражэ зи ши ноапте, ка сэ не апере ымпотрива ловитурилор лор.
10 Pa nthawi yomweyi anthu a ku Yuda anati, “Mphamvu za anthu onyamula zinyalala zikutha ndipo pali zinyalala zambiri. Choncho ife sititha kumanga khomali.”
Ынсэ Иуда зичя: „Путериле челор че дук повериле слэбеск ши дэрымэтуриле сунт мулте; ну вом путя сэ зидим зидул.”
11 Adani athunso anati, “Iwo asanadziwe izi, kapena kutiona, tidzakhala tili pakati pawo ndipo tidzawapha ndi kuyimitsa ntchitoyo.”
Ши врэжмаший ноштри зичяу: „Ну вор шти ши ну вор ведя нимик пынэ вом ажунӂе ын мижлокул лор; ый вом учиде ши вом фаче астфел сэ ынчетезе лукраря.”
12 Ndipo Ayuda amene ankhala pafupi ndi adani athuwo anabwera kakhumi konse kuchokera konse kumene ankakhala kudzatiwuza kuti tibwereko ku ntchito.
Ши иудеий каре локуяу лынгэ ей ау венит де зече орь ши не-ау ынштиинцат деспре тоате локуриле пе унде веняу ла ной.
13 Choncho kumbuyo kwa khoma, cha mʼmunsi mwake komanso malo amene anali asanathe ndinayikamo anthu mʼmabanja atatenga malupanga, mikondo ndi mauta awo.
Де ачея ам пус ын локуриле челе май де жос, динапоя зидулуй, ши ын локуриле тарь, попорул пе фамилий, й-ам ашезат пе тоць ку сэбииле, сулицеле ши аркуриле лор.
14 Popeza anthu ankachita mantha, tsono ndinawawuza anthu olemekezeka, akuluakulu ndiponso anthu onse kuti, “Musawaope. Kumbukirani kuti Ambuye ndi wamkulu ndipo ndi woopsa. Choncho menyerani nkhondo abale anu, ana aamuna ndi aakazi, akazi anu ndi nyumba zanu.”
М-ам уйтат ши, скулынду-мэ, ам зис май-марилор, дрегэторилор ши челуйлалт попор: „Ну вэ темець де ей! Адучеци-вэ аминте де Домнул чел маре ши ынфрикошат ши луптаць пентру фраций воштри, пентру фиий воштри ши фетеле воастре, пентру невестеле воастре ши пентру каселе воастре!”
15 Adani athu atamva kuti ife tadziwa za chiwembu chawo, anadziwanso kuti Yehova walepheretsa zimene ankafuna kutichita. Choncho tinabwerera aliyense ku ntchito yake yomanga khoma.
Кынд ау аузит врэжмаший ноштри кэ ам фост ынштиинцаць, Думнезеу ле-а нимичит планул ши не-ам ынторс ку тоций ла зид, фиекаре ла лукраря луй.
16 Kuyambira tsiku limenelo mpaka mʼtsogolo mwake, theka la antchito anga linkagwira ntchito, pamene theka linalo limatenga mikondo, zishango, mauta ndi kuvala malaya azitsulo. Akuluakulu ankalimbikitsa Ayuda onse
Дин зиуа ачея, жумэтате дин оамений мей лукрау, яр чялалтэ жумэтате ера ынарматэ ку сулице, ку скутурь, ку аркурь ши ку платоше. Кэпетенииле ерау ынапоя ынтреӂий касе а луй Иуда.
17 amene ankamanga khoma. Anthu onyamula zinyalala aja ankagwira ntchito ndi dzanja limodzi, dzanja linali atanyamula chida chankhondo.
Чей че зидяу зидул ши чей че дучяу сау ынкэркау повериле ку о мынэ лукрау, яр ку алта циняу арма.
18 Mʼmisiri aliyense ankamangirira lupanga lake mʼchiwuno mwake akamagwira ntchito. Koma munthu woyimba lipenga anali pambali panga nthawi zonse.
Фиекаре дин ей, кынд лукра, ышь авя сабия ынчинсэ ла мижлок. Чел че суна дин трымбицэ стэтя лынгэ мине.
19 Ndipo ine ndinati kwa anthu olemekezeka ndi anthu ena onse, “Ntchitoyi ndi yayikulu ndipo ili padera lalikulu ndipo ifeyo takhala motayanatayana kwambiri pa khoma.
Ам зис май-марилор, дрегэторилор ши челуйлалт попор: „Лукраря есте маре ши ынтинсэ, ши ной сунтем рисипиць пе зид, департе уний де алций.
20 Tsono kulikonse kumene muliko, mukamva kulira kwa lipenga bwerani mudzasonkhane kumene kuli ine kuno. Mulungu wathu adzatimenyera nkhondo.”
Ла сунетул трымбицей сэ вэ стрынӂець ла ной, спре локул де унде о вець аузи. Думнезеул ностру ва лупта пентру ной.”
21 Choncho enafe tinapitiriza kugwira ntchito, pamene theka lina linkanyamula mikondo kuyambira mʼbandakucha mpaka nyenyezi zitaoneka.
Аша фэчям лукраря: жумэтате дин ной стынд ку сулица ын мынэ дин зорий зилей пынэ ла ивиря стелелор.
22 Pa nthawi imeneyo ndinawuzanso anthuwo kuti, “Aliyense pamodzi ndi wantchito wake agone mu Yerusalemu kuti tikhale ndi otilondera usiku ndi kuti masana tizigwira ntchito.”
Ын ачелашь тимп, ам май зис попорулуй: „Фиекаре сэ петрякэ ноаптя ын Иерусалим ку служиторул луй; ноаптя сэ фачем де стражэ, яр зиуа сэ лукрэм.”
23 Choncho ine, anzanga, antchito anga, ndi anthu otiteteza amene ankanditsata panalibe ndi mmodzi yemwe anavula zovala zake pogona. Aliyense anasunga chida chake chankhondo pambali pake.
Ши ну не-ам дезбрэкат де хайне, нич еу, нич фраций мей, нич служиторий мей, нич оамений де стражэ, каре ерау суб порунка мя. Фиекаре се дучя ку армеле ла апэ.

< Nehemiya 4 >