< Nehemiya 4 >
1 Sanibalati atamva kuti tikumanganso khoma anapsa mtima nayamba kuseka ndi kunyogodola Ayuda kwambiri.
Kane Sanbalat owinjo ni wasechako gero ohinga, iye nowangʼ kendo mirima nomake. Ne ojaro jo-Yahudi,
2 Ndipo anayankhula pamaso pa abale ake ndi asilikali a Samariya kuti, “Kodi Ayuda ofowokawa akuchita chiyani? Kodi iwo nʼkumanganso khoma? Kodi adzaperekanso nsembe? Kodi adzatsiriza ntchitoyi tsiku limodzi? Kodi adzachita kutenga miyala yakale ija ndi mmene inapseramo?”
e nyim joma ne giriworego kod jolweny mag jo-Samaria, mowachonegi niya, “En angʼo ma jo-Yahudi manyapgi timo ka? Bende gibiro chako gero ohingano? Bende gibiro chiwo misango? Bende gibiro tieke godiechiengʼ achiel? Bende gibiro miyo kitegi bedo mangima ka gia e pith mag yugigo, kaka owangʼ-gi malichni?”
3 Tobiya wa ku Amoni, amene anali naye anati, “Chimene akumangacho ngati nkhandwe itakwerapo, itha kugwetsa khoma lawolo!”
Tobia ma ja-Amon, mane ochungʼ e bathe, nowacho niya, “Ohinga ma gigerono, kata ka kibwe ema oidho, to obiro ruombore piny!”
4 Tsono ndinayamba kupemphera kuti, “Timvereni, Inu Mulungu wathu, mmene akutinyozera. Mulole kuti mawu awo onyoza awabwerere, ndipo atengedwe ukapolo ku dziko lachilendo.
Winjwa, yaye Nyasachwa, nimar osejarwa. Mad idwok ayenjegi e wigi giwegi. Mad ichiwgi kaka wasumbini e piny mabor ka joma oter e twech.
5 Musawakhululukire mphulupulu zawo kapena kufafaniza machimo awo pamaso panu popeza aputa ukali wanu pamaso pa anthu omanga khoma.”
Kik ium gigo magisetimo ma ok odhi kare kata iruch richogi e nyim wangʼi, nimar gisediro ayenje e wangʼ jogedo.
6 Choncho ife tinamangabe khomalo kufikira lonse litafika theka la msinkhu wake, chifukwa chakuti anthu anagwira ntchitoyo ndi mtima wawo wonse.
Omiyo ne wagero ohinga nyaka ne ochopo nus mar borne, nikech ji notiyo gi chunygi duto.
7 Koma pamene Sanibalati, Tobiya, Aarabu, Aamoni ndi anthu a ku Asidodi anamva kuti ntchito yokonzanso makoma a Yerusalemu ikupitirirabe ndipo kuti mipata ikutsekedwa, anapsa mtima kwambiri.
To ka Sanbalat, Tobia, jo-Arabu, jo-Amon kod jo-Ashdod nowinjo ni loso ohinga mar Jerusalem osedhi nyime to kendo ni kuonde motuch ne idino, igi nowangʼ ahinya.
8 Tsono onse anapangana za chiwembu kuti abwere ndi kudzathira nkhondo anthu a ku Yerusalemu ndi kuyambitsa mapokoso pakati pawo.
Negichokore giduto mondo gibi giked gi Jerusalem kendo gimi ji obed gi luoro.
9 Koma ife tinapemphera kwa Mulungu wathu ndipo tinayika alonda otiteteza kwa adaniwo usiku ndi usana.
To ne walamo Nyasachwa mi waketo jorito odiechiengʼ gotieno mondo gigengʼ kihondkoni.
10 Pa nthawi yomweyi anthu a ku Yuda anati, “Mphamvu za anthu onyamula zinyalala zikutha ndipo pali zinyalala zambiri. Choncho ife sititha kumanga khomali.”
Kuom mano, jo-Juda nowacho niya, “Pidhe mag kuonde momukore ngʼeny, to teko joma gologi odok chien, omiyo koro ok wanyal dhi nyime gigero ohinga.”
11 Adani athunso anati, “Iwo asanadziwe izi, kapena kutiona, tidzakhala tili pakati pawo ndipo tidzawapha ndi kuyimitsa ntchitoyo.”
Wasikwa bende nowacho niya, “Ka pod ok gi ngʼeyo kata ka pod ok gi nenowa, to wabiro poree e diergi kendo wabiro negogi mi wachung tich.”
12 Ndipo Ayuda amene ankhala pafupi ndi adani athuwo anabwera kakhumi konse kuchokera konse kumene ankakhala kudzatiwuza kuti tibwereko ku ntchito.
Bangʼe jo-Yahudi mane odak mokiewo kodgi nobiro kendo okonewa nyadipar niya, “Gibiro monjou kamoro ma udhiyoe.”
13 Choncho kumbuyo kwa khoma, cha mʼmunsi mwake komanso malo amene anali asanathe ndinayikamo anthu mʼmabanja atatenga malupanga, mikondo ndi mauta awo.
Emomiyo ne aketo jomoko e tok ohinga kuonde modok gi piny ma ginyalo nenogo wasigu ka aketogi dala ka dala, ka gin-gi ligengni, tonge kod atungʼ.
14 Popeza anthu ankachita mantha, tsono ndinawawuza anthu olemekezeka, akuluakulu ndiponso anthu onse kuti, “Musawaope. Kumbukirani kuti Ambuye ndi wamkulu ndipo ndi woopsa. Choncho menyerani nkhondo abale anu, ana aamuna ndi aakazi, akazi anu ndi nyumba zanu.”
Kane asenono gigi maber, ne achungo malo kendo awachone joka ruoth, jotelo kod joma moko niya, “Kik uluorgi. Par Ruoth Nyasaye, maduongʼ kendo malich, kendo ukedne oweteu, yawuotu kod nyiu, mondeu, kod miechu.”
15 Adani athu atamva kuti ife tadziwa za chiwembu chawo, anadziwanso kuti Yehova walepheretsa zimene ankafuna kutichita. Choncho tinabwerera aliyense ku ntchito yake yomanga khoma.
Ka wasikwa nowinjo ni wasefwenyo chenro margi kendo ni Nyasaye ne oseketho parogi, ne wadok wate e gero ohinga, ngʼato ka ngʼato e tichne.
16 Kuyambira tsiku limenelo mpaka mʼtsogolo mwake, theka la antchito anga linkagwira ntchito, pamene theka linalo limatenga mikondo, zishango, mauta ndi kuvala malaya azitsulo. Akuluakulu ankalimbikitsa Ayuda onse
Kochakore e odiechiengno, nus mar joga notiyo tijno, to nus modongʼ nomanore gi tongʼ, okumba, atungʼ kod gige lweny mag akor. Jotelo nochungʼ e tok jo-Juda duto
17 amene ankamanga khoma. Anthu onyamula zinyalala aja ankagwira ntchito ndi dzanja limodzi, dzanja linali atanyamula chida chankhondo.
mane gero ohinga. Joma ne otingʼo gige gedo ne tiyo gi lwetgi, to lwetgi komachielo otingʼo gir lweny,
18 Mʼmisiri aliyense ankamangirira lupanga lake mʼchiwuno mwake akamagwira ntchito. Koma munthu woyimba lipenga anali pambali panga nthawi zonse.
to jagedo ka jagedo notingʼo liganglane e bathe kodhi nyime kod tich. To ngʼatno mane goyo turumbete nodongʼ koda.
19 Ndipo ine ndinati kwa anthu olemekezeka ndi anthu ena onse, “Ntchitoyi ndi yayikulu ndipo ili padera lalikulu ndipo ifeyo takhala motayanatayana kwambiri pa khoma.
Bangʼe ne awachone joka ruoth, jotelo kod joma moko niya, “Tich ngʼeny kendo pek, to wangelore e kor ohingani.
20 Tsono kulikonse kumene muliko, mukamva kulira kwa lipenga bwerani mudzasonkhane kumene kuli ine kuno. Mulungu wathu adzatimenyera nkhondo.”
Kamoro amora ma uwinjo ka turumbete oywakie, to yworwauru kanyo. Nyasachwa biro kedonwa!”
21 Choncho enafe tinapitiriza kugwira ntchito, pamene theka lina linkanyamula mikondo kuyambira mʼbandakucha mpaka nyenyezi zitaoneka.
Omiyo ne wadhi nyime gi tich ka nus mar jowa otingʼo tongʼ, kochakore kogwen nyaka sa ma piny imore.
22 Pa nthawi imeneyo ndinawuzanso anthuwo kuti, “Aliyense pamodzi ndi wantchito wake agone mu Yerusalemu kuti tikhale ndi otilondera usiku ndi kuti masana tizigwira ntchito.”
E sechego ne awachone ji niya, “Ket ngʼato ka ngʼato kod jakonyne obed ei Jerusalem gotieno, mondo omi gibed jorito gotieno, to giti godiechiengʼ.”
23 Choncho ine, anzanga, antchito anga, ndi anthu otiteteza amene ankanditsata panalibe ndi mmodzi yemwe anavula zovala zake pogona. Aliyense anasunga chida chake chankhondo pambali pake.
An, kata owetena kata joga kata jorit mane ni koda ne ok ogolo lepgi; moro ka moro notingʼo liganglane mar lweny, kata mana ka wadhi tuomo pi.