< Nehemiya 3 >

1 Pambuyo pake Eliyasibu mkulu wa ansembe ndi ansembe anzake anayamba kugwira ntchito ndipo anamanganso Chipata cha Nkhosa. Iwo anachipatulira Mulungu ndipo anayika zitseko zake. Khoma limene analipatula linafika mpaka pa Nsanja ya Zana ndi Nsanja ya Hananeli.
Ket timmakder ni Eliasib a kangatoan a padi agraman dagiti kakabsatna a padi ket binangonda ti Ruangan ti Karnero. Kinonsagrarda daytoy ket inkabilda dagiti ruanganna. Kinonsagrarda daytoy agingga iti Torre dagiti Sangagasut ken agingga iti Torre ni Hananel.
2 Anthu a ku Yeriko anamanga chigawo china pambali pake ndipo Zakuri mwana wa Imuri anamanga chigawo chinanso choyandikana nawo.
Simmaruno kenkuana a nagtrabaho dagiti lallaki ti Jerico ken simmaruno kadakuada a nagtrabaho ni Zaccur a putot ni Imri.
3 Chipata cha Nsomba chinamangidwanso ndi ana a fuko la Hasena. Iwo anayika mitanda yake ndi zitseko, zotsekera zake, ndi mipiringidzo yake.
Imbangon dagiti putot ni Hassenaa ti Ruangan ti Lames. Inkabilda dagiti awanan iti pakaikabilanda, inkabilda dagiti ruanganna, dagiti pagbalunetanna ken dagiti balunetna.
4 Meremoti mwana wa Uriya, mwana wa Hakozi, anakonza chigawo choyandikana nacho. Motsatana naye, Mesulamu mwana wa Berekiya, mwana wa Mesezabeli anakonza chigawo china. Pambali pake, Zadoki mwana wa Baana anakonzanso chigawo china.
Tinarimaan ni Meremot ti sumaruno a paset. Isuna ket putot ni Urias a putot ni Hakkoz. Ket simmaruno kadakuada a nagtarimaan ni Mesullam. Isuna ket putot ni Barakias a putot ni Mesezabel. Simmaruno kadakuada a nagtarimaan ni Zadok. Isuna ket putot ni Baana.
5 Pambali pa iwowa anthu a ku Tekowa anakonza chigawo china. Koma wolemekezeka awo anakana kugwira ntchito imene akuluakulu awo anawapatsa.
Simmaruno kadakuada a nagtarimaan dagiti taga-Tekoa, ngem nagkedked dagiti panguloenda a mangaramid iti imbilin dagiti mangimatmaton kadakuada.
6 Chipata cha Yesana chinakonzedwa ndi Yoyada mwana wa Paseya ndi Mesulamu mwana wa Besodeya. Iwo anayika mitanda yake ndi kuyika zitseko, zotsekera zake ndi mipiringidzo yake.
Tinarimaan da Joyada a putot ni Pasea ken Mesullam a putot ni Besodias ti Daan a Ruangan. Inkabilda dagiti awanan, dagiti ridawna, dagiti pagbalunetanna ken dagiti balunetna.
7 Pambali pawo Melatiya Mgibeyoni ndi Yadoni Mmerenoti ndiponso anthu a ku Gibiyoni ndi a ku Mizipa anakonza chigawo chawo mpaka ku nyumba ya bwanamkubwa wa chigawo cha Patsidya pa Yufurate.
Simmaruno kadakuada a nagtarimaan ni Melatias a taga-Gabaon, kaduana ni Jadon a taga-Meronot. Indadauloanda dagiti lallaki ti Gabaon ken Mizpa. Ti Mizpa ket nagnaedan ti gobernador iti probinsia iti ballasiw ti Karayan.
8 Pambali pawo Uzieli mwana wa Harihaya wa mʼgulu amisiri osula golide anakonzanso chigawo china. Pambali pake Hananiya mmodzi mwa anthu oyenga mafuta onunkhira, anakonzanso chigawo china. Iwo anakonzanso Yerusalemu mpaka ku Khoma Lotambasuka.
Simmaruno kenkuana a nagtarimaan ni Uzziel, a putot ni Harhaias, a maysa kadagiti mammanday iti balitok, ken simmaruno kenkuana ni Hananias nga agar-aramid iti bangbanglo. Imbangonda manen ti Jerusalem agingga iti Akaba a Pader.
9 Refaya mwana wa Huri wolamulira theka la chigawo cha Yerusalemu anakonza chigawo china motsatana nawo.
Simmaruno kadakuada a nagtarimaan ni Refaias a putot ni Hur. Isuna ti mangiturturay iti kagudua a distrito ti Jerusalem.
10 Kulumikiza ichi, Yedaya mwana wa Harumafi anakonza chigawo choyangʼanana ndi nyumba yake, ndipo Hatusi mwana wa Hasabaneya anakonzanso motsatana naye.
Simmaruno kadakuada, tinarimaan ni Jedaias a putot ni Harumaf ti abay ti balayna. Simmaruno kenkuana a nagtarimaan ni Hattus a putot ni Hasabneyas.
11 Malikiya mwana wa Harimu ndi Hasubu mwana wa Pahati-Mowabu anakonzanso chigawo china ndiponso Nsanja ya Ngʼanjo.
Tinarimaan da Malkija a putot ni Harim ken Hassub a putot ni Pahat Moab ti maysa pay a paset ken ti Torre dagiti Urno.
12 Salumu mwana wa Halohesi wolamulira theka la chigawo cha Yerusalemu, anakonzanso chigawo chotsatana nawo mothandizidwa ndi ana ake akazi.
Simmaruno kadakuada a nagtarimaan ni Sallum, a putot ni Hallohes, a mangiturturay iti kagudua a distrito ti Jerusalem, agraman dagiti annakna a babbai.
13 Chipata cha ku chigwa chinakonzedwa ndi Hanuni ndi anthu okhala ku Zanowa. Iwo anachimanganso ndi kuyika zitseko zake ndi zotsekera ndi mipiringidzo yake. Iwo anakonzanso khoma lotalika mamita 450 mpaka ku Chipata cha Zinyalala.
Tinarimaan ni Hanun ken dagiti agnanaed iti Zanoa ti Ruangan ti Tanap. Imbangonda daytoy ken inkabilda dagiti ruanganna, dagiti pagibalunetanna ken dagiti balunetna. Tinarimaanda ti pader a sangaribu a kubiko ti kaatiddogna agingga iti Ruangan a Pagiruaran iti Rugit.
14 Chipata cha Zinyalala chinakonzedwa ndi Malikiya mwana wa Rekabu, wolamulira chigawo cha Beti-Hakeremu. Iye anachimanganso ndi kuyika zitseko zake, zotsekera zake ndi mipiringidzo.
Tinarimaan ni Malkija, a putot ni Rekab, a mangiturturay iti distrito ti Bet Hakkerem ti Ruangan a Pagiruaran iti Rugit. Imbangonna daytoy ket inkabilna dagiti ridawna, dagiti pagbalunetanna ken dagiti balunetna.
15 Chipata cha Kasupe chinakonzedwa ndi Saluni mwana wa Koli-Hoze, wolamulira chigawo cha Mizipa. Iye anachimanganso ndi kuyikanso denga ndiponso zitseko, zotsekera ndi mipiringidzo yake. Iye anakonzanso khoma la Dziwe la Siloamu limene lili pafupi ndi munda wa mfumu mpaka ku makwerero otsikira potuluka mzinda wa Davide.
Imbangon manen ni Sallum, a putot ni Colhoze, a mangiturturay iti distrito ti Mizpa ti Ruangan ti Burayok. Imbangonna daytoy, inatepanna ken inkabilna dagiti ruanganna, dagiti pagibalunetanna ken dagiti balunetna. Imbangonna pay ti pader iti Tangke ti Siloam iti abay ti hardin ti ari, agingga iti agdan nga agpababa manipud iti siudad ni David.
16 Pambali pa iyeyo, Nehemiya mwana wa Azibuki, wolamulira theka la chigawo cha Beti Zuri anakonza chigawo china mpaka kumalo oyangʼanana ndi manda a Davide, mpaka ku dziwe lokumba ndi ku nyumba ya anthu ankhondo.
Tinarimaan ni Nehemias, a putot ni Azbuk, a mangiturturay iti kagudua a distrito ti Bet-zur, ti paset a batog dagiti tanem ni David, agingga iti naaramid a tangke ken agingga iti balay dagiti mamaingel a lallaki.
17 Pambali pake Alevi anakonza chigawo china, ndipo mtsogoleri wawo anali Rehumi mwana wa Bani. Pambali pa iye Hasabiya wolamulira theka la chigawo cha Keyila anagwira ntchito ku chigawo chake.
Simmaruno kenkuana a nagtarimaan dagiti Levita, pakairamanan ni Rehum a putot ni Bani ken simmaruno kenkuana a nagtarimaan iti masakupanna ni Hasabias a mangiturturay iti kagudua a distrito ti Keila.
18 Pambuyo pa iyeyu abale awo anapitiriza kukonza, ndipo mtsogoleri wawo anali Bawai mwana wa Henadadi, wolamulira theka lina la chigawo cha Keyila.
Simmaruno kenkuana a nagtarimaan dagiti kailianda, pakairamanan ni Bavvai, a putot ni Henadad, a mangiturturay iti kagudua a distrito ti Keila.
19 Motsatana naye Ezeri mwana wa Yesuwa, wolamulira Mizipa anakonza chigawo chinanso choyangʼanana ndi chikweza chofikira ku nyumba yosungira zida za nkhondo pa ngodya.
Simmaruno kenkuana a nagtarimaan ni Ezer, a putot ni Jesua, a mangiturturay iti Mizpa. Tinarimaanna ti sabali a paset iti batog ti sang-atan nga agturong iti pagiduldulinan iti armas, iti pagsikkoan.
20 Motsatana naye, Baruki mwana wa Zakai anakonzanso chigawo china kuchokera pa ngodya mpaka pa chitseko cha nyumba ya Eliyasibu mkulu wa ansembe.
Simmaruno kenkuana, sireregget a tinarimaan ni Baruc a putot ni Zabbai ti sabali pay a paset, manipud iti pagsikkoan agingga iti ruangan iti balay ni Eliasib a kangatoan a padi.
21 Motsatana naye, Meremoti mwana wa Uriya, mwana wa Hakozi anakonzanso chigawo china kuchokera ku chitseko cha nyumba ya Eliyasibu mpaka kumapeto kwake.
Simmaruno kenkuana, tinarimaan ni Meremot a putot ni Urias a putot ni Hakkoz ti sabali pay a paset, manipud iti ruangan ti balay ni Eliasib agingga iti pungto ti balay ni Eliasib.
22 Pambuyo pake ansembe okhala ku chidikha anakonzanso chigawo china.
Simmaruno kenkuana a nagtarimaan dagiti padi, isuda dagiti lallaki a naggapu iti aglawlaw ti Jerusalem.
23 Pambuyo pawo, Benjamini ndi Hasubu anakonza kutsogolo kwa nyumba zawo. Ndipo motsatana nawo, Azariya mwana wa Maaseya mwana wa Ananiya, anakonza chigawo choyangʼanana ndi nyumba zawo.
Simmaruno kadakuada, tinarimaan da Benjamin ken Hassub ti batog ti balayda. Simmaruno kadakuada, tinarimaan ni Azarias a putot ni Maasias a putot ni Ananias ti abay ti balayna.
24 Motsatana naye, Binuyi mwana wa Henadadi anakonzanso chigawo china, kuchokera pa nyumba ya Azariya kukafika potsirizira pa ngodya.
Simmaruno kenkuana, tinarimaan ni Binnui a putot ni Henadad ti sabali pay a paset, manipud iti balay ni Azarias agingga iti pagsikkoan.
25 Palali mwana Uzai anakonza chigawo china choyangʼanana ndi ngodya ndi nsanja yotuluka pa nyumba yapamwamba ya mfumu ku bwalo la alonda. Motsatana naye, Pedaya mwana wa Parosi,
Tinarimaan ni Palal a putot ni Uzai ti sangoanan ti pagsikkoan ken ti torre nga agpangato manipud iti akin-ngato a balay ti ari idiay paraangan ti guardia. Simmaruno kenkuana a nagtarimaan ni Pedaias a putot ni Paros.
26 ndi otumikira mʼNyumba ya Mulungu amene amakhala pa khoma la Ofeli anakonza chigawo china mpaka pa malo oyangʼanana ndi Chipata cha Madzi kuloza kummawa ndiponso nsanja yayitali ija.
Ita, tinarimaan dagiti adipen iti templo nga agnanaed idiay Ofel ti paset iti batog ti Ruangan ti Danum iti daya ti torre a pagguardiaan iti templo.
27 Motsatana nawo, anthu a ku Tekowa anakonzanso chigawo china choyangʼanana ndi nsanja ija yayikulu ndi yayitali mpaka ku khoma la Ofeli.
Simmaruno kenkuana, tinarimaan dagiti taga-Tekoa ti sabali pay a paset, iti batog ti nakangatngato a torre, agingga iti pader ti Ofel.
28 Kuyambira ku Chipata cha Akavalo anakonza ndi ansembe ena ndipo aliyense amakonza khoma loyangʼanana ndi nyumba yake.
Nagtarimaan dagiti padi iti ngatoen ti Ruangan ti Kabalio, iti tunggal batog ti balayda.
29 Motsatana nawo, Zadoki mwana wa Imeri anakonza chigawo china choyangʼanana ndi nyumba yake. Motsatana naye, Semeya mwana wa Sekaniya, mlonda wa Chipata cha Kummawa, anakonzanso khoma.
Simmaruno kadakuada, tinarimaan ni Zadok a putot ni Immer ti paset iti batog ti balayna. Ket simmaruno kenkuana a nagtarimaan ni Semaias, a putot ni Secanias, a mangay-aywan iti akindaya a ruangan.
30 Hananiya mwana wa Selemiya ndiponso Hanuni mwana wachisanu ndi chimodzi wa Zalafi anakonza chigawo china. Motsatana naye, Mesulamu mwana wa Berekiya anakonza chigawo choyangʼanana ndi chipinda chake.
Simmaruno kenkuana, tinarimaan da Hananias a putot ni Selemias ken Hanun a maikainnem a putot ni Zalaf ti sabali pay a paset. Simmaruno kenkuana, tinarimaan ni Mesullam a putot ni Barakias ti batog ti pagnanaedanna.
31 Motsatana naye, Malikiya mmodzi mwa amisiri a golide anakonza chigawo china mpaka ku nyumba ya atumiki a ku Nyumba ya Mulungu ndiponso ku nyumba ya anthu amalonda moyangʼanana ndi chipata cha Mifikade ndiponso mpaka pa chipinda chapamwamba chapangodya.
Simmaruno kenkuana, tinarimaan ni Malkija a maysa kadagiti mammanday iti balitok, ti paset agingga iti balay dagiti agserserbi iti templo ken dagiti agtagtagilako iti batog ti Ruangan nga Agturong iti Templo ken ti akin-ngato a pagnanaedan a kuarto iti suli.
32 Ndipo pakati pa chipinda chapamwamba chapangodya ndi Chipata cha Nkhosa anakonza ndi amisiri a golide ndi anthu amalonda.
Tinarimaan dagiti mammanday iti balitok ken dagiti agtagtagilako ti nagbaetan ti akin-ngato a kuarto iti suli ken ti Ruangan ti Karnero.

< Nehemiya 3 >