< Nehemiya 13 >
1 Pa tsiku limenelo anawerenga buku la Mose anthu akumva. Ndipo anapeza mawu akuti, Mwamoni kapena Mmowabu asalowe konse mu msonkhano wa Mulungu.
Tai dienā Mozus grāmatā lasīja priekš ļaužu ausīm un tur atrada rakstītu, ka Amoniešiem un Moabiešiem ne mūžam nebūs nākt Dieva draudzē,
2 Paja iwowa sanawachingamire Aisraeli kukawapatsa chakudya ndi madzi. Mʼmalo mwake analemba ganyu Baalamu kuti adzawatemberere. Komabe Mulungu wathu anasandutsa tembererolo kukhala mdalitso.
Tāpēc ka viņi nebija nākuši pretī Israēla bērniem ar maizi un ar ūdeni, bet pret tiem bija derējuši Bileāmu, viņus nolādēt, lai gan mūsu Dievs lāstu pārvērta par svētību.
3 Anthu atamva lamuloli, anachotsa pakati pawo onse amene anali achilendo.
Tad notikās, ka šo bauslību dzirdot tie visus svešiniekus atšķīra no Israēla.
4 Izi zisanachitike, wansembe Eliyasibu anali atasankhidwa kukhala woyangʼanira zipinda zosungiramo katundu za Nyumba ya Mulungu. Iyeyu ankagwirizana kwambiri ndi Tobiya.
Un priesteris Elijašibs, kas bija iecelts pār mūsu Dieva nama kambari, papriekš bija sadraudzējies ar Tobiju,
5 Choncho anamupatsa chipinda chachikulu chimene kale ankasungamo zopereka zakudya, lubani, ziwiya, zopereka za chakhumi za tirigu, vinyo ndi mafuta zoyenera kuperekedwa kwa Alevi, oyimba nyimbo ndi alonda a ku Nyumba ya Mulungu, komanso mphatso zoyenera kupereka kwa ansembe.
Un viņam bija taisījis lielu kambari, kur tie papriekš bija nolikuši ēdamo upuri, vīraku un rīkus un labības, vīna un eļļas desmitos, kas kļuva nodoti priekš levitiem un dziedātājiem un vārtu sargiem, līdz ar priesteru cilājamo upuri.
6 Koma pamene izi zonse zinkachitika mu Yerusalemu, ine kunalibe popeza mʼchaka cha 32 cha Aritasasita mfumu ya Babuloni ine ndinabwerera kwa mfumu. Patapitanso nthawi ndinapempha chilolezo kwa mfumuyo
Bet viss tas notika, kamēr es Jeruzālemē nebiju; jo Artakserksus, Bābeles ķēniņa, trīsdesmit otrā gadā es nācu pie ķēniņa, un pēc kāda laika es to no ķēniņa izlūdzos.
7 ndipo ndinabwerera ku Yerusalemu. Kumeneko ndinamva za chinthu choyipa chimene Eliyasibu anachita pomupatsa Tobiya chipinda mʼbwalo la Nyumba ya Mulungu.
Kad es nu nācu uz Jeruzālemi un samanīju to ļaunumu, ko Elijašibs priekš Tobijas bija darījis, viņam kambari taisīdams Dieva nama pagalmos,
8 Ndinapsa mtima kwambiri ndipo ndinataya kunja katundu yense wa Tobiya amene anali mʼchipindamo.
Tad tas man ļoti rieba, un es izmetu visas Tobijas nama lietas no tā kambara ārā.
9 Ndinalamulira kuti ayeretse zipinda, ndipo kenaka ndinabwezeramo zida za mʼNyumba ya Mulungu, pamodzi ndi chopereka cha zakudya ndi lubani.
Es arī pavēlēju, to kambari šķīstīt, un es atkal tur ienesu Dieva nama rīkus ar ēdamo upuri un vīraku.
10 Ndinapezanso kuti Alevi sankalandira magawo awo amene amayera kulandira. Chotsatira chake Alevi onse pamodzi ndi oyimba nyimbo amene ankagwira ku Nyumba ya Mulungu anathawa, aliyense kupita ku munda wake.
Es arī samanīju, ka levitiem viņu daļa nebija dota, tā ka leviti un dziedātāji, kas to darbu darījuši, bija aizmukuši ikkatrs uz savu tīrumu.
11 Choncho ndinadzudzula akuluakulu aja ndipo ndinawafunsa kuti, “Nʼchifukwa chiyani Nyumba ya Mulungu yasiyidwa?” Ndipo ine ndinawayitanitsa pamodzi ndi kuwayika mʼmalo awo.
Tad es bāros ar tiem virsniekiem un sacīju: kāpēc Dieva nams ir atstāts? Un es tos sapulcināju un tos atkal iecēlu viņu vietā.
12 Pambuyo pake Ayuda anayambanso kubwera ndi zopereka zawo za chakhumi cha tirigu, vinyo ndi mafuta kuti ziperekedwe ku nyumba yosungiramo chuma.
Tad visa Jūda valsts atnesa to desmito no labības un no vīna un no eļļas mantas namos.
13 Ndipo ndinasankha wansembe Selemiya, mlembi Zadoki, ndi Mlevi wotchedwa Pedaya kukhala oyangʼanira zipinda zosungiramo. Ndinasankhanso Hanani mwana wa Zakuri mwana wa Mataniya kukhala wowathandizira chifukwa ndinaona kuti anthu awa anali odalirika. Ntchito yawo inali yogawira abale awo zinthu zofunika.
Un es par mantu sargiem iecēlu priesteri Šelemiju un rakstu mācītāju Cadoku un Pedaju no levitiem, un viņiem pa roku Hananu, Zakura, Matanijas dēla, dēlu; jo šie tapa turēti par uzticamiem, un tiem tapa uzlikts, lai izdala saviem brāļiem.
14 Inu Mulungu wanga, mundikumbukire pa zimenezi, ndipo musafafanize ntchito zanga zimene ndachita mokhulupirika pa Nyumba yanu pofuna kukutumikirani.
Piemini mani, mans Dievs, par to un neizdeldē manu labdarīšanu, ko esmu darījis pie sava Dieva nama un pie viņa kalpošanas!
15 Nthawi imeneyo ndinaona anthu a mu Yuda akuponda ndi kufinya mphesa pa tsiku la Sabata. Ena ankawunjika tirigu milumilu ndi kumasenzetsa abulu. Enanso ankabwera ndi vinyo, mphesa, mkuyu ndi katundu wa mitundumitundu ku Yerusalemu pa tsiku la Sabata. Choncho ndinawachenjeza za kugulitsa zakudya pa tsiku la Sabata.
Tanīs dienās es Jūdā redzēju, ka vīna spaidus mina svētā dienā, un ka kūlīšus saņēma, ko uz ēzeļiem krāva, vīnu, vīna ķekarus un vīģes un visādu nastu, un svētā dienā ienesa Jeruzālemē, un es tai dienā (pret tiem) devu liecību, kad tie barību pārdeva.
16 Nawonso anthu a ku Turo amene ankakhala mu Yerusalemu ankabweretsa nsomba ndi akatundu ena onse amalonda kudzagulitsa pa Sabata kwa anthu a mʼdziko la Yuda ndi a mu Yerusalemu.
Tur arī Tirieši dzīvoja, kas zivis atnesa un visādu preci, un to pārdeva svētā dienā Jūda bērniem un Jeruzālemē.
17 Ndipo ndinadzudzula anthu olemekezeka a dziko la Yuda. Ndinawafunsa kuti, “Nʼchoyipa chanji mukuchitachi, kumayipitsa tsiku la Sabata chotere?
Tad es bāros ar Jūda virsniekiem un uz tiem sacīju: kas tas par ļaunu darbu, ko jūs darāt un pārkāpjat svēto dienu?
18 Makolo anu anachita zomwezi ndipo Mulungu wathu anadzetsa mavuto pa ife ndi pa mzinda uwu. Kodi inu mukufuna kuwutsanso mkwiyo wa Mulungu pa Israeli pamene mukudetsa tsiku la Sabata?”
Vai jūsu tēvi tā nav darījuši, un mūsu Dievs ir vedis visu šo nelaimi pār mums un pār šo pilsētu? Un jūs vairojiet tās dusmas pār Israēli, pārkāpdami svēto dienu!
19 Nʼchifukwa chake ndikulamula kuti pamene kuyamba kuda, tsiku la Sabata lisanayambe, azitseka zipata zonse za Yerusalemu ndipo asazitsekule mpaka sabata litatha. Ndinayika ena mwa antchito anga oyangʼanira pa zipata kuti katundu aliyense asalowe mu Yerusalemu pa tsiku la Sabata.
Un notikās svētai dienai nākot, kad tumšs metās Jeruzālemes vārtos, tad es pavēlēju durvis aizslēgt un neatdarīt, kamēr svētā diena pagājusi. Un no saviem puišiem es kādus liku pie vārtiem, ka nekādu nastu tur neienestu svētā dienā.
20 Choncho kamodzi kapena kawiri anthu amalonda ndi anthu ogulitsa katundu osiyanasiyana ankagona usiku wonse kunja kwa Yerusalemu.
Tad tie zāļu un visādas preces pārdevēji palika pa nakti ārā Jeruzālemes priekšā vienreiz un otrreiz.
21 Koma ndinawachenjeza ndi kuwafunsa kuti, “Nʼchifukwa chiyani mukugona pafupi ndi khoma? Ngati muchitanso zimenezi, ine ndidzakugwirani.” Kuyambira nthawi imeneyo, sanabwerenso pa tsiku la Sabata.
Un es pret tiem apliecināju un uz tiem sacīju: kāpēc jūs pa nakti paliekat pie mūra? Ja jūs to atkal darīsiet, tad es jūs grābšu rokā. No tā laika tie vairs nenāca svētā dienā.
22 Ndipo ndinalamulira Alevi kuti adziyeretse okha ndi kubwera kudzalonda pa zipata ndi cholinga choti tsiku la Sabata likhale tsiku loyera. Inu Mulungu wanga, kumbukireninso ine pa zimenezi ndipo mundisunge malingana ndi chikondi chanu chachikulu chosasinthika.
Un levitiem es sacīju, lai šķīstās un nāk vārtus sargāt, ka svētā diena taptu svētīta. Arī par to piemini mani, mans Dievs, un žēlo mani pēc Tavas lielās žēlastības!
23 Masiku amenewo ndinaonanso anthu a ku Yuda amene anakwatira akazi ochokera ku Asidodi, Amoni ndi Mowabu.
Es tanīs dienās arī redzēju Jūdus, kas bija apņēmuši Ašdodiešu, Amoniešu un Moabiešu sievas.
24 Theka la ana awo linkayankhula chiyankhulo cha Asidodi kapena chiyankhulo chimodzi cha anthu ena, ndipo sankathanso kuyankhula chiyankhulo cha Ayuda.
Un viņu bērni runāja pus Ašdodiski un nemācēja Jūdiski runāt, bet pēc abēju tautu valodas.
25 Tsono ndinakangana nawo ndi kuwatemberera. Ndinamenya ena mwa anthuwo ndi kuzula tsitsi lawo. Ine ndinawalumbiritsa mʼdzina la Mulungu kuti, “Inu musapereke ana anu aakazi kuti akwatiwe ndi ana awo aamuna kapena inuyo ngakhale ana anu aamuna kukwatira ana awo aakazi.
Tad es ar tiem bāros un tos lādēju un situ kādus no tiem un tiem plūcu matus un tiem liku pie Dieva zvērēt, jums nebūs savas meitas dot viņu dēliem, nedz ņemt viņu meitas saviem dēliem nedz sev.
26 Kodi Solomoni mfumu ya Israeli suja anachimwa chifukwa cha ukwati ngati umenewu. Pakati pa mitundu yambiri panalibe mfumu ngati iyi. Iye anakondedwa ndi Mulungu wake, ndipo Mulungu anamuyika kukhala mfumu ya Israeli yense, koma iyeyo anachimwa chifukwa cha akazi achilendo.
Vai šo dēļ Salamans, Israēla ķēniņš, nav apgrēkojies? Jebšu nevienai tautai tāds ķēniņš nav bijis, kāds viņš bija, un viņš savam Dievam bija mīļš, un Dievs viņu bija iecēlis par ķēniņu pār visu Israēli, un tomēr ir tādu tās svešās sievas paveda uz grēkiem.
27 Kodi tsopano ife tizimva inu kuti mukuchita choyipa chachikulu chimenechi, kupandukira Yehova Mulungu wathu pomakwatira akazi achilendo?”
Vai tad mēs jums klausīsim un visu tādu lielu ļaunumu darīsim noziegdamies pret savu Dievu, ka apņemam svešas sievas?
28 Mmodzi mwa ana aamuna a Yehoyada mwana Eliyasibu mkulu wa ansembe nʼkuti nthawi imeneyi ali mpongozi wa Sanibalati wa ku Horoni. Choncho ndinamuthamangitsa pamaso panga.
Un viens no Jojada, Elijašiba dēla, tā augstā priestera, bērniem bija par znotu palicis Sanebalatam, tam Horonietim, tāpēc es viņu aizdzinu no sevis projām.
29 Inu Mulungu wanga, mukumbukire mmene iwo anayipitsira unsembe, pangano la unsembe komanso la Alevi.
Piemini viņus, mans Dievs, tāpēc ka tie sagānījuši priesteru amatu un priesteru un levitu derību!
30 Motero ndinayeretsa ansembe ndi Alevi powachotsera kalikonse kachilendo. Ndipo ndinakhazikitsa ntchito zawo, kuti aliyense akhale pa ntchito yake.
Tā es tos šķīstīju no visiem svešiem ieradumiem un noliku priesteriem un levitiem, ikkatram savu darīšanu savā kalpošanā,
31 Ndiponso kupereka nkhuni ndi zipatso zoyamba kucha pa nthawi yake. Ndikumbukireni pondikomera mtima, Inu Mulungu wanga.
Un to malkas došanu noliktos laikos un tos pirmajus. Piemini, mans Dievs, man to par labu!