< Nehemiya 11 >

1 Nthawi imeneyo atsogoleri a anthu ankakhala ku Yerusalemu. Tsono anthu ena onse anachita maere kuti apeze munthu mmodzi pa anthu khumi aliwonse kuti azikhala ku Yerusalemu, mzinda wopatulika. Anthu asanu ndi anayi otsalawo ankakhala mʼmidzi yawo.
سران قوم در شهر مقدّس اورشلیم ساکن شدند. از سایر مردم نیز یک دهم به قید قرعه انتخاب شدند تا در اورشلیم ساکن شوند و بقیه در شهرهای دیگر سکونت گزیدند.
2 Anthu anayamikira onse amene anadzipereka kuti azikhala mu Yerusalemu.
در ضمن، کسانی که داوطلبانه به اورشلیم می‌آمدند تا در آنجا زندگی کنند مورد ستایش مردم قرار می‌گرفتند.
3 Aisraeli wamba, ansembe, Alevi, ogwira ntchito ku Nyumba ya Mulungu ndiponso zidzukulu za antchito a Solomoni ankakhala mʼmidzi yawo, aliyense mu dera lake. Koma atsogoleri a chigawo cha Yuda anali atakhazikika mu Yerusalemu.
سایر مردم همراه عده‌ای از کاهنان، لاویان، خدمتگزاران خانۀ خدا و نسل خادمان سلیمان پادشاه در املاک اجدادی خود در شهرهای دیگر یهودا باقی ماندند،
4 Ku Yerusalemu kunkakhalanso anthu ena a mafuko a Yuda ndi Benjamini. Ena mwa zidzukulu za Yuda ndi awa: Ataya, mwana wa Uziya, mwana wa Zekariya, mwana wa Amariya mwana wa Sefatiya, mwana wa Mahalaleli. Onsewa anali ana a Perezi.
اما برخی از مردم یهودا و بنیامین در اورشلیم ساکن شدند. از قبیلهٔ یهودا: عتایا (عتایا پسر عزیا، عزیا پسر زکریا، زکریا پسر امریا، امریا پسر شفطیا، شفطیا پسر مهلل‌ئیل و مهلل‌ئیل از نسل فارص بود)؛
5 Ena ndi awa: Maaseya mwana wa Baruki, mwana wa Koli-Hoze mwana wa Hazaya, mwana wa Adaya, mwana wa Yowaribu, Zekariya mwana wa Msiloni.
معسیا (معسیا پسر باروک، باروک پسر کُلحوزِه، کُلحوزِه پسر حزیا، حزیا پسر عدایا، عدایا پسر یویاریب، یویاریب پسر زکریا، و زکریا پسر شیلونی بود).
6 Zidzukulu zonse za Perezi, anthu amphamvu zawo amene ankakhala ku Yerusalemu analipo anthu okwanira 468.
جمعاً ۴۶۸ نفر از بزرگان نسل فارص در اورشلیم زندگی می‌کردند.
7 Nazi zidzukulu za Benjamini: Salu mwana wa Mesulamu, mwana wa Yowedi, mwana wa Pedaya, mwana wa Kolaya, mwana wa Maaseiya, mwana wa Itieli, mwana wa Yesaiya.
از قبیلهٔ بنیامین: سلو (سلو پسر مشلام، مشلام پسر یوعید، یوعید پسر فدایا، فدایا پسر قولایا، قولایا پسر معسیا، معسیا پسر ایتی‌ئیل، ایتی‌ئیل پسر اشعیا بود)؛ جبای و سلای. جمعاً ۹۲۸ نفر از قبیلهٔ بنیامین در اورشلیم زندگی می‌کردند. سردستهٔ ایشان یوئیل پسر زکری و معاون او یهودا پسر هسنواه بود.
8 Abale ake anali Gabayi ndi Salaya. Onse pamodzi anali 928.
9 Yoweli mwana wa Zikiri ndiye anali mtsogoleri wawo, ndipo Yuda mwana wa Hasenuya ndiye amayangʼanira chigawo cha chiwiri cha mzinda.
10 Ansembe anali awa: Yedaya mwana wa Yowaribu; Yakini;
از کاهنان: یدعیا (پسر یویاریب)؛ یاکین؛ سرایا (سرایا پسر حلقیا، حلقیا پسر مشلام، مشلام پسر صادوق، صادوق پسر مرایوت، و مرایوت پسر اخیطوب کاهن اعظم بود). افراد این طایفه که جمعاً ۸۲۲ نفر می‌شدند در خانهٔ خدا خدمت می‌کردند. عدایا (عدایا پسر یروحام، یروحام پسر فللیا، فللیا پسر امصی، امصی پسر زکریا، زکریا پسر فشحور و فشحور پسر ملکیا بود). افراد این طایفه جمعاً ۲۴۲ نفر بودند و از سران خاندانها محسوب می‌شدند. عمشیسای (عمشیسای پسر عزرئیل، عزرئیل پسر اخزای، اخزای پسر مشلیموت، مشلیموت پسر امیر بود). افراد این طایفه ۱۲۸ نفر بودند و همگی جنگجویان شجاعی به شمار می‌آمدند. ایشان زیر نظر زبدی‌ئیل (پسر هجدولیم) خدمت می‌کردند.
11 Seraya mwana wa Hilikiya mwana wa Mesulamu, mwana wa Zadoki, mwana wa Merayoti, mwana wa Ahitubi amene anali woyangʼanira Nyumba ya Mulungu,
12 ndi abale awo, amene ankagwira ntchito ku Nyumba ya Mulungu. Onse pamodzi anali 822. Panalinso Adaya mwana wa Yerohamu, mwana wa Pelaliya, mwana wa Amizi, mwana wa Zekariya, mwana wa Pasi-Huri, mwana wa Malikiya,
13 ndi abale ake, amene anali atsogoleri a mabanja. Onse pamodzi anali 242. Kuphatikiza apo panalinso Amasisai mwana wa Azaireli, mwana wa Ahazayi, mwana wa Mesilemoti, mwana wa Imeri
14 ndi abale ake. Onse pamodzi anali 128 ndipo anali anthu olimba mtima kwambiri. Mtsogoleri wawo wamkulu anali Zabidieli mwana wa Hagedolimu.
15 Alevi anali awa: Semaya mwana wa Hasubu, mwana wa Azirikamu, mwana wa Hasabiya, mwana wa Buni.
از لاویان: شمعیا (شمعیا پسر حشوب، حشوب پسر عزریقام، عزریقام پسر حشبیا، حشبیا پسر بونی بود)؛ شبتای و یوزاباد (دو نفر از سران لاویان بودند و کارهای خارج از خانهٔ خدا را انجام می‌دادند)؛ متنیا (متنیا پسر میکا، میکا پسر زبدی و زبدی پسر آساف بود) او سردستهٔ سرایندگان خانۀ خدا بود و مراسم پرستش را رهبری می‌کرد؛ بقبقیا (معاون متنیا)؛ عبدا (عبدا پسر شموع، شموع پسر جلال و جلال پسر یِدوتون بود).
16 Sabetayi ndi Yozabadi anali atsogoleri amene ankayangʼanira ntchito ya kunja kwa Nyumba ya Mulungu.
17 Mataniya mwana wa Mika, mwana wa Zabidi, mwana wa Asafu ndiye anali wotsogolera pa mapemphero achiyamiko. Panalinso Bakibukiya amene anali wachiwiri pakati pa abale ake. Kuwonjezera apo panalinso Abida mwana wa Samuwa, mwana wa Galali, mwana wa Yedutuni.
18 Alevi onse amene anali mu mzinda woyera analipo 284.
روی هم ۲۸۴ لاوی در شهر مقدّس اورشلیم زندگی می‌کردند.
19 Alonda a ku Nyumba ya Mulungu anali awa: Akubu, Talimoni ndi abale awo. Onse pamodzi anali 172.
از نگهبانان: عقوب، طلمون و بستگان ایشان که جمعاً ۱۷۲ نفر بودند.
20 Aisraeli ena onse pamodzi ndi ansembe ndi Alevi ankakhala mʼmizinda ya Yuda, ndipo aliyense ankakhala mʼdera la makolo ake.
سایر کاهنان و لاویان و بقیهٔ قوم اسرائیل در املاک اجدادی خود در شهرهای دیگر یهودا ماندند.
21 Koma antchito a ku Nyumba ya Mulungu ankakhala pa phiri la Ofeli, ndipo Ziha ndi Gisipa ndiwo anali kuwayangʼanira.
خدمتگزاران خانهٔ خدا (که سرپرستان ایشان صیحا و جشفا بودند) در بخشی از اورشلیم به نام عوفل زندگی می‌کردند.
22 Wamkulu wa Alevi mu Yerusalemu anali Uzi mwana wa Bani, mwana wa Hasabiya, mwana wa Mataniya, mwana wa Mika. Uzi anali mmodzi wa zidzukulu za Asafu, amene anali oyimba nyimbo pa nthawi zachipembedzo mʼNyumba ya Mulungu.
سرپرست لاویان اورشلیم که در خانهٔ خدا خدمت می‌کردند عزی بود. (عزی پسر بانی، بانی پسر حشبیا، حشبیا پسر متنیا، متنیا پسر میکا و میکا از نسل آساف بود. سرایندگان خانهٔ خدا از طایفهٔ آساف بودند.)
23 Pakuti mfumu inalamula kuti tsiku ndi tsiku pa nthawi zachipembedzo oyimba nyimbowo azikhalapo.
خدمت روزانهٔ دستهٔ سرایندگان طبق مقرراتی که از دربار وضع شده بود، تعیین می‌شد.
24 Petahiya mwana wa Mesezabeli, mmodzi mwa zidzukulu za Zera mwana wa Yuda ndiye ankayimirira Aisraeli pa bwalo la mfumu ya Perisiya.
فتحیا (پسر مشیزبئیل، از نسل زارح پسر یهودا) نمایندهٔ مردم اسرائیل در دربار پادشاه پارس بود.
25 Anthu ena a fuko la Yuda ankakhala ku Kiriyati-Ariba ndi midzi yake, ku Diboni ndi midzi yake, ku Yekabizeeli ndi midzi yake,
شهرها و روستاهای دیگری که مردم یهودا در آنها زندگی می‌کردند، عبارت بودند از: قریه اربع، دیبون، یقبصی‌ئیل و روستاهای اطراف آنها؛ یشوع، مولاده، بیت‌فالط، حصرشوعال، بئرشبع و روستاهای اطراف آن؛ صقلغ، مکونه و روستاهای اطراف آن؛ عین رمون، صرعه، یرموت، زانوح، عدلام و روستاهای اطراف آنها؛ لاکیش و نواحی اطراف آن، عزیقه و روستاهای اطراف آن. به این ترتیب مردم یهودا در ناحیهٔ بین بئرشبع و دره هنوم زندگی می‌کردند.
26 ku Yesuwa, Molada, Beti-Peleti,
27 Hazari-Suwali, Beeriseba ndi midzi yawo.
28 Ku Zikilagi, Mekona ndi midzi yawo,
29 ku Eni-Rimoni, Zora, Yarimuti,
30 Zanowa, Adulamu ndi midzi yake, ku Lakisi ndi minda yake, ku Beeriseba mpaka ku chigwa cha Hinomu.
31 Nazonso zidzukulu za Benjamini zinkakhala mʼdera lawo kuyambira ku Geba mpaka ku Mikimasi, Ayiya, Beteli ndi midzi yake,
اهالی قبیلهٔ بنیامین در این شهرها سکونت داشتند: جبع، مکماش، عیا، بیت‌ئیل و روستاهای اطراف آن؛ عناتوت، نوب، عننیه، حاصور، رامه، جتایم، حادید، صبوعیم، نبلاط، لود، اونو و دره صنعتگران.
32 ku Anatoti, Nobu ndi Ananiya,
33 ku Hazori, Rama ndi Gitaimu,
34 ku Hadidi, Zeboimu ndi Nebalati,
35 ku Lodi, Ono ndi ku chigwa cha Amisiri.
36 Magulu ena a Alevi a ku Yuda ankakhala ku Benjamini.
بعضی از لاویان که در سرزمین یهودا بودند، به سرزمین بنیامین فرستاده شدند تا در آنجا ساکن شوند.

< Nehemiya 11 >