< Nehemiya 11 >

1 Nthawi imeneyo atsogoleri a anthu ankakhala ku Yerusalemu. Tsono anthu ena onse anachita maere kuti apeze munthu mmodzi pa anthu khumi aliwonse kuti azikhala ku Yerusalemu, mzinda wopatulika. Anthu asanu ndi anayi otsalawo ankakhala mʼmidzi yawo.
Ja kansan päämiehet asuivat Jerusalemissa; mutta muu kansa heitti arpaa, saattaaksensa yhden kymmenestä asumaan Jerusalemiin, siihen pyhään kaupunkiin, mutta yhdeksän osaa kaupungeissa.
2 Anthu anayamikira onse amene anadzipereka kuti azikhala mu Yerusalemu.
Ja kansa siunasi kaikkia niitä miehiä, jotka mielistyivät asumaan Jerusalemissa.
3 Aisraeli wamba, ansembe, Alevi, ogwira ntchito ku Nyumba ya Mulungu ndiponso zidzukulu za antchito a Solomoni ankakhala mʼmidzi yawo, aliyense mu dera lake. Koma atsogoleri a chigawo cha Yuda anali atakhazikika mu Yerusalemu.
Nämä ovat maakunnan päämiehet, jotka asuivat Jerusalemissa; mutta Juudan kaupungeissa asui itsekukin omaisuuudessansa kaupungeissansa: Israel, papit, Leviläiset, Netinimit ja Salomon palveliain lapset.
4 Ku Yerusalemu kunkakhalanso anthu ena a mafuko a Yuda ndi Benjamini. Ena mwa zidzukulu za Yuda ndi awa: Ataya, mwana wa Uziya, mwana wa Zekariya, mwana wa Amariya mwana wa Sefatiya, mwana wa Mahalaleli. Onsewa anali ana a Perezi.
Ja Jerusalemissa asuivat muutamat Juudan ja Benjaminin lapsista. Juudan lapsista: Ataja Ussian poika, Sakarian pojan, Amarian pojan, Sephatian pojan, Mahalaleelin pojan, Peretsen lapsista,
5 Ena ndi awa: Maaseya mwana wa Baruki, mwana wa Koli-Hoze mwana wa Hazaya, mwana wa Adaya, mwana wa Yowaribu, Zekariya mwana wa Msiloni.
Ja Maeseja Barukin poika, Kolhosen pojan, Hasajan pojan, Adajan pojan, Jojaribin pojan, Sakarian pojan, Silomin pojan,
6 Zidzukulu zonse za Perezi, anthu amphamvu zawo amene ankakhala ku Yerusalemu analipo anthu okwanira 468.
Kaikki Peretsen lapset, jotka asuivat Jerusalemissa, neljäsataa ja kahdeksanseitsemättäkymmentä vahvaa miestä.
7 Nazi zidzukulu za Benjamini: Salu mwana wa Mesulamu, mwana wa Yowedi, mwana wa Pedaya, mwana wa Kolaya, mwana wa Maaseiya, mwana wa Itieli, mwana wa Yesaiya.
Nämät olivat Benjaminin lapset: Sallu Mesullamin poika, Joedin pojan, Pedajan pojan, Kolajan pojan, Maasejan pojan, Itielin pojan, Jesajan pojan;
8 Abale ake anali Gabayi ndi Salaya. Onse pamodzi anali 928.
Ja hänen jälkeensä Gabbai, Sallai, yhdeksänsataa ja kahdeksankolmattakymmentä;
9 Yoweli mwana wa Zikiri ndiye anali mtsogoleri wawo, ndipo Yuda mwana wa Hasenuya ndiye amayangʼanira chigawo cha chiwiri cha mzinda.
Ja Joel Sikrin poika oli heidän esimiehensä, ja Juuda Senuan poika oli toisena kaupungin päällä.
10 Ansembe anali awa: Yedaya mwana wa Yowaribu; Yakini;
Papeista, Jedaja Jojaribin poika, Jakin,
11 Seraya mwana wa Hilikiya mwana wa Mesulamu, mwana wa Zadoki, mwana wa Merayoti, mwana wa Ahitubi amene anali woyangʼanira Nyumba ya Mulungu,
Seraja Hilkian poika, Mesullamin pojan, Zadokin pojan, Merajotin pojan, Ahitobin pojan, Jumalan huoneen päämies,
12 ndi abale awo, amene ankagwira ntchito ku Nyumba ya Mulungu. Onse pamodzi anali 822. Panalinso Adaya mwana wa Yerohamu, mwana wa Pelaliya, mwana wa Amizi, mwana wa Zekariya, mwana wa Pasi-Huri, mwana wa Malikiya,
Ja heidän veljiänsä, jotka huoneessa työtä tekivät, oli kahdeksansataa ja kaksikolmattakymmentä; ja Adaja Jerohamin poika, Pelalian pojan, Amsin pojan, Sakarian pojan, Pashurin pojan, Malkian pojan,
13 ndi abale ake, amene anali atsogoleri a mabanja. Onse pamodzi anali 242. Kuphatikiza apo panalinso Amasisai mwana wa Azaireli, mwana wa Ahazayi, mwana wa Mesilemoti, mwana wa Imeri
Ja hänen veljensä isäin päämiehet kaksisataa ja kaksiviidettäkymmentä; ja Amasia Asareelin poika, Ahasain pojan, Mesillemotin pojan, Immerin pojan,
14 ndi abale ake. Onse pamodzi anali 128 ndipo anali anthu olimba mtima kwambiri. Mtsogoleri wawo wamkulu anali Zabidieli mwana wa Hagedolimu.
Ja heidän veljensä, väkevät miehet, sata ja kahdeksankolmattakymmentä; ja Sabdiel Gedolimin poika oli heidän esimiehensä.
15 Alevi anali awa: Semaya mwana wa Hasubu, mwana wa Azirikamu, mwana wa Hasabiya, mwana wa Buni.
Leviläisistä: Semaja Hasubin poika, Asrikamin pojan, Hasabian pojan, Bunnin pojan;
16 Sabetayi ndi Yozabadi anali atsogoleri amene ankayangʼanira ntchito ya kunja kwa Nyumba ya Mulungu.
Ja Sabtai ja Josabad, Leviläisten päämiehistä, Jumalan huoneen ulkonaisessa työssä;
17 Mataniya mwana wa Mika, mwana wa Zabidi, mwana wa Asafu ndiye anali wotsogolera pa mapemphero achiyamiko. Panalinso Bakibukiya amene anali wachiwiri pakati pa abale ake. Kuwonjezera apo panalinso Abida mwana wa Samuwa, mwana wa Galali, mwana wa Yedutuni.
Ja Mattania Miikan poika, Sabdin pojan, Asaphin pojan, joka oli ylimmäinen kiitosta alkamaan rukouksessa; ja Bakbukia toinen veljeinsä keskellä, ja Abda Sammuan poika, Galalin pojan, Jedutunin pojan.
18 Alevi onse amene anali mu mzinda woyera analipo 284.
Leviläisiä oli kaikkiansa pyhässä kaupungissa kaksisataa ja neljäyhdeksättäkymmentä;
19 Alonda a ku Nyumba ya Mulungu anali awa: Akubu, Talimoni ndi abale awo. Onse pamodzi anali 172.
Ja ovenvartiat: Akkub, Talmon ja heidän veljensä, jotka porteissa vartioitsivat, sata ja kaksikahdeksattakymmentä.
20 Aisraeli ena onse pamodzi ndi ansembe ndi Alevi ankakhala mʼmizinda ya Yuda, ndipo aliyense ankakhala mʼdera la makolo ake.
Mutta muut Israelista, papit ja Leviläiset olivat kaikissa Juudan kaupungeissa, jokainen omassa perinnössänsä.
21 Koma antchito a ku Nyumba ya Mulungu ankakhala pa phiri la Ofeli, ndipo Ziha ndi Gisipa ndiwo anali kuwayangʼanira.
Ja Netinimit asuivat Ophelissa: ja Ziha ja Gispa olivat Netinimein päällä.
22 Wamkulu wa Alevi mu Yerusalemu anali Uzi mwana wa Bani, mwana wa Hasabiya, mwana wa Mataniya, mwana wa Mika. Uzi anali mmodzi wa zidzukulu za Asafu, amene anali oyimba nyimbo pa nthawi zachipembedzo mʼNyumba ya Mulungu.
Mutta Leviläisten esimies oli Jerusalemissa, Ussi Banin poika, Hasabian pojan, Mattanian pojan, Miikan pojan; veisaajat olivat Asaphin pojista, Jumalan huoneen työn tykönä.
23 Pakuti mfumu inalamula kuti tsiku ndi tsiku pa nthawi zachipembedzo oyimba nyimbowo azikhalapo.
Sillä se oli kuninkaan käsky heille, että veisaajille piti oleman päiväinen määrä.
24 Petahiya mwana wa Mesezabeli, mmodzi mwa zidzukulu za Zera mwana wa Yuda ndiye ankayimirira Aisraeli pa bwalo la mfumu ya Perisiya.
Ja Petaja Mesesabeelin poika Seran lapsista, Juudan pojan, oli kuninkaan käskyläinen kaikissa asioissa kansan tykö.
25 Anthu ena a fuko la Yuda ankakhala ku Kiriyati-Ariba ndi midzi yake, ku Diboni ndi midzi yake, ku Yekabizeeli ndi midzi yake,
Ja Juudan lapset, ne jotka ulkona olivat kylissä heidän maassansa; muutamat asuivat Kirjatarbassa ja sen kylissä, ja Dibonissa ja sen kylissä, ja Kabseelissa ja sen kylissä,
26 ku Yesuwa, Molada, Beti-Peleti,
ja Jesuassa, Moladassa, Betpaletissa,
27 Hazari-Suwali, Beeriseba ndi midzi yawo.
Ja Hasarsualissa, Bersebassa ja sen kylissä,
28 Ku Zikilagi, Mekona ndi midzi yawo,
Ja Ziklagissa ja Mekonassa ja sen kylissä,
29 ku Eni-Rimoni, Zora, Yarimuti,
Ja Enrimmonissa, Zorgassa, Jarmutissa,
30 Zanowa, Adulamu ndi midzi yake, ku Lakisi ndi minda yake, ku Beeriseba mpaka ku chigwa cha Hinomu.
Zanoassa, Adullamissa ja sen kylissä, Lakiksessa ja sen kedolla Asekassa ja sen kylissä. Ja he oleskelivat hamasta Bersebasta niin Hinnomin laaksoon asti.
31 Nazonso zidzukulu za Benjamini zinkakhala mʼdera lawo kuyambira ku Geba mpaka ku Mikimasi, Ayiya, Beteli ndi midzi yake,
Mutta Benjaminin lapset Gabaasta asuivat Mikmassa, Ajassa ja Betelissä ja niiden kylissä,
32 ku Anatoti, Nobu ndi Ananiya,
Anatotissa, Nobissa, Ananiassa,
33 ku Hazori, Rama ndi Gitaimu,
Hatsorissa, Ramassa, Gittaimissa,
34 ku Hadidi, Zeboimu ndi Nebalati,
Hadidissa, Ziboimissa, Neballatissa,
35 ku Lodi, Ono ndi ku chigwa cha Amisiri.
Lodissa ja Onossa, Seppäin laaksossa.
36 Magulu ena a Alevi a ku Yuda ankakhala ku Benjamini.
Ja muutamat Leviläiset asuivat Juudan ja Benjaminin rajoilla.

< Nehemiya 11 >