< Nehemiya 10 >

1 Amene anasindikiza chidindo anali awa: Nehemiya, bwanamkubwa uja, mwana wa Hakaliya. Zedekiya,
Följande namn stodo på skrivelserna som buro sigillen: Nehemja, ståthållaren, Hakaljas son, och Sidkia,
2 Seraya, Azariya, Yeremiya
Seraja, Asarja, Jeremia,
3 Pasuri, Amariya, Malikiya,
Pashur, Amarja, Malkia,
4 Hatusi, Sebaniya, Maluki,
Hattus, Sebanja, Malluk,
5 Harimu, Meremoti, Obadiya,
Harim, Meremot, Obadja,
6 Danieli, Ginetoni, Baruki,
Daniel, Ginneton, Baruk,
7 Mesulamu, Abiya, Miyamini
Mesullam, Abia, Mijamin,
8 Maziya, Biligai ndi Semaya Awa anali ansembe.
Maasja, Bilgai, Semaja; dessa voro prästerna.
9 Alevi anali awa: Yesuwa mwana wa Azaniya, Binuyi wa fuko la Henadadi, Kadimieli,
Och leviterna voro: Jesua, Asanjas son, Binnui, av Henadads barn, Kadmiel,
10 ndi abale awo awa: Sebaniya, Hodiya, Kelita, Pelaya, Hanani,
så ock deras bröder: Sebanja, Hodia, Kelita, Pelaja, Hanan,
11 Mika, Rehobu, Hasabiya,
Mika, Rehob, Hasabja,
12 Zakuri, Serebiya, Sebaniya,
Sackur, Serebja, Sebanja,
13 Hodiya, Bani ndi Beninu.
Hodia, Bani och Beninu.
14 Atsogoleri a anthu anali awa: Parosi, Pahati-Mowabu, Elamu, Zatu, Bani,
Folkets huvudmän voro: Pareos, Pahat-Moab, Elam, Sattu, Bani,
15 Buni, Azigadi, Bebai,
Bunni, Asgad, Bebai,
16 Adoniya, Bigivai, Adini,
Adonia, Bigvai, Adin,
17 Ateri, Hezekiya, Azuri,
Ater, Hiskia, Assur,
18 Hodiya, Hasumu, Bezayi
Hodia, Hasum, Besai,
19 Harifu, Anatoti, Nebayi,
Harif, Anatot, Nobai,
20 Magipiyasi, Mesulamu, Heziri
Magpias, Mesullam, Hesir,
21 Mesezabeli, Zadoki, Yaduwa
Mesesabel, Sadok, Jaddua,
22 Pelatiya, Hanani, Ananiya,
Pelatja, Hanan, Anaja,
23 Hoseya, Hananiya, Hasubu
Hosea, Hananja, Hassub,
24 Halohesi, Piliha, Sobeki,
Hallohes, Pilha, Sobek,
25 Rehumu, Hasabiya, Maaseya,
Rehum, Hasabna, Maaseja,
26 Ahiya, Hanani, Anani,
Ahia, Hanan, Anan,
27 Maluki, Harimu ndi Baana.
Malluk, Harim och Baana.
28 Ife otsalafe, ndiye kuti ansembe, Alevi, alonda a ku Nyumba ya Mulungu, oyimba nyimbo, ogwira ntchito ku Nyumba ya Mulungu, onse amene anadzipatula pakati pa anthu a mitundu ina kuti atsate malamulo a Yehova, pamodzi ndi akazi athu, ana athu ndi onse amene ali ndi nzeru,
Och det övriga folket, prästerna, leviterna, dörrvaktarna, sångarna, tempelträlarna och alla de som hade avskilt sig från de främmande folken och vänt sig till Guds lag, så ock deras hustrur, söner och döttrar, alla som hade kommit till moget förstånd,
29 tikuphatikana ndi abale athu wolemekezeka, ndipo tikulonjeza molumbira kuti tidzayenda motsata malamulo a Mulungu amene anapereka kudzera mwa Mose mtumiki wa Mulungu. Tilonjeza kumvera ndi kutsata bwino mawu onse, miyambo yonse ndi malangizo onse a Yehova. Yehova atilange ngati sitidzachita zimenezi.
dessa slöto sig till sina förnämligare bröder och gingo ed och svuro att de skulle vandra efter Guds lag, den som hade blivit given genom Guds tjänare Mose, och att de skulle hålla och göra efter alla HERRENS, vår HERRES, bud och rätter och stadgar,
30 “Ife tikulonjeza kuti sitidzapereka ana athu aakazi kuti akwatiwe ndi amuna a mayiko ena kapena kutenga ana awo aakazi kuti akwatiwe ndi ana athu aamuna.
att vi icke skulle giva våra döttrar åt de främmande folken, ej heller taga deras döttrar till hustrur åt våra söner.
31 “Ngati anthu a mitundu ina abwera ndi zinthu za malonda, monga tirigu, kudzagulitsa pa tsiku la Sabata, sitidzawagula pa tsiku la Sabata kapena pa tsiku lina lililonse loyera. Pa chaka chilichonse cha chisanu ndi chiwiri tidzagoneka munda wosawulima ndipo tidzafafaniza ngongole zonse.
Och när de främmande folken förde in handelsvaror eller något slags säd till salu på sabbatsdagen, skulle vi icke köpa det av dem på sabbat eller helgdag; och vi skulle låta vart sjunde år vara friår och då avstå från alla slags krav.
32 “Tikulonjezanso molumbira kuti chaka ndi chaka tizipereka magalamu anayi a siliva kuti zithandize ntchito ya ku Nyumba ya Mulungu wathu.
Och vi fastställde för oss den förpliktelsen att såsom vår gärd årligen erlägga en tredjedels sikel till tjänsten i vår Guds hus,
33 Ndalamayi izithandiza kulipirira buledi wa pa tebulo, chopereka cha chakudya cha nthawi zonse, zopereka zopsereza za nthawi zonse, zopereka za pa tsiku la Sabata, za pachikondwerero cha Mwezi Watsopano, za pa masiku a chikondwerero osankhika, zopereka za zinthu zopatulika, zopereka za nsembe yopepesera machimo a Aisraeli ndi ntchito ina iliyonse ya ku Nyumba ya Mulungu.
nämligen till skådebröden, och till det dagliga brännoffret, och till offren på sabbaterna, vid nymånaderna och högtiderna, och till tackoffren, och till syndoffren för Israels försoning, och till allt arbete i vår Guds hus.
34 “Ife ansembe, Alevi ndi anthu onse, tachita maere kuti tidziwe pamene banja lathu lililonse lidzabweretsa ku nyumba ya Mulungu wathu pa nthawi yoyikika ya chaka zopereka za nkhuni zoyaka pa guwa lansembe la Yehova Mulungu wathu, monga momwe zinalembedwera mʼMalamulo.”
Och vi, prästerna, leviterna och folket, kastade lott angående vedoffret, huru man årligen skulle föra det till vår Guds hus på bestämda tider, efter våra familjer, för att antändas på HERRENS, vår Guds, altare, såsom det är föreskrivet i lagen.
35 “Tilonjezanso kuti tidzabwera ndi zipatso zoyamba kucha za mʼminda yathu ndi zipatso zoyamba kucha za mtengo uliwonse wa zipatso chaka ndi chaka kuti tidzapereke ku Nyumba ya Mulungu wathu.”
Och vi skulle årligen föra till HERRENS hus förstlingen av vår mark, och förstlingen av all frukt på alla slags träd,
36 “Tidzabweranso nawo ku Nyumba ya Mulungu, kwa ansembe amene amatumikira ku Nyumba ya Mulungu ana athu aamuna oyamba kubadwa ndi ana angʼombe oyamba kubadwa monga zalembedwera mu Malamulo. Tidzaperekanso ana oyamba kubadwa a ziweto zathu ndi ana ankhosa oyamba kubadwa.”
och de förstfödda av våra söner och av vår boskap, såsom det är föreskrivet i lagen; vi skulle föra till vår Guds hus de förstfödda både av våra fäkreatur och av vår småboskap, till prästerna som gjorde tjänst i vår Guds hus.
37 “Ndiponso ku zipinda za Nyumba ya Mulungu wathu, kwa ansembe tidzaperekanso mtanda wathu wa buledi wa ufa ndi mphatso zina monga zipatso za mtengo uliwonse, vinyo ndi mafuta. Tidzaperekanso kwa alevi chakhumi cha mbewu zathu pakuti alevi ndiwo amasonkhanitsa chakhumi mʼmidzi yathu yonse.
Och förstlingen av vårt mjöl och våra offergärder, så ock av allt slags trädfrukt, av vin och olja skulle vi föra till prästerna, in i kamrarna i vår Guds hus, och tionden av vår jord till leviterna; ty det var leviterna som skulle uppbära tionden i alla de städer vid vilka vi brukade jorden.
38 Wansembe, mdzukulu wa Aaroni azikhala pamodzi ndi Alevi pamene akulandira chakhumi. Ndipo Alevi azibwera ndi chakhumicho ku nyumba ya Mulungu wathu, kuzipinda zosungiramo chuma.”
Och en präst, en av Arons söner, skulle vara med leviterna, när leviterna uppburo tionden; och själva skulle leviterna föra tionden av sin tionde upp till vår Guds hus, in i förrådshusets kamrar.
39 Choncho Israeli, kuphatikiza zidzukulu za Alevi, azipititsa zopereka za tirigu, vinyo ndi mafuta ku zipinda zosungiramo katundu wopatulika, komanso kokhala ansembe amene akutumikira pamodzi ndi alonda a ku Nyumba ya Mulungu ndi anthu oyimba nyimbo. “Kwambiri ife sitidzaleka kusamala Nyumba ya Mulungu.”
Ty såväl de övriga israeliterna som Levi barn skulle föra sin offergärd av säd, vin och olja in i dessa kamrar, där helgedomens kärl och de tjänstgörande prästerna, ävensom dörrvaktarna och sångarna voro. Alltså skulle vi icke försumma vår Guds hus.

< Nehemiya 10 >