< Nehemiya 10 >

1 Amene anasindikiza chidindo anali awa: Nehemiya, bwanamkubwa uja, mwana wa Hakaliya. Zedekiya,
and upon [the] to seal Nehemiah [the] governor son: child Hacaliah and Zedekiah
2 Seraya, Azariya, Yeremiya
Seraiah Azariah Jeremiah
3 Pasuri, Amariya, Malikiya,
Pashhur Amariah Malchijah
4 Hatusi, Sebaniya, Maluki,
Hattush Shebaniah Malluch
5 Harimu, Meremoti, Obadiya,
Harim Meremoth Obadiah
6 Danieli, Ginetoni, Baruki,
Daniel Ginnethon Baruch
7 Mesulamu, Abiya, Miyamini
Meshullam Abijah Mijamin
8 Maziya, Biligai ndi Semaya Awa anali ansembe.
Maaziah Bilgai Shemaiah these [the] priest
9 Alevi anali awa: Yesuwa mwana wa Azaniya, Binuyi wa fuko la Henadadi, Kadimieli,
and [the] Levi and Jeshua son: child Azaniah Binnui from son: child Henadad Kadmiel
10 ndi abale awo awa: Sebaniya, Hodiya, Kelita, Pelaya, Hanani,
and brother: male-relative their Shebaniah Hodiah Kelita Pelaiah Hanan
11 Mika, Rehobu, Hasabiya,
Mica Rehob Hashabiah
12 Zakuri, Serebiya, Sebaniya,
Zaccur Sherebiah Shebaniah
13 Hodiya, Bani ndi Beninu.
Hodiah Bani Beninu
14 Atsogoleri a anthu anali awa: Parosi, Pahati-Mowabu, Elamu, Zatu, Bani,
head: leader [the] people Parosh Pahath-moab Pahath-moab Elam Zattu Bani
15 Buni, Azigadi, Bebai,
Bunni Azgad Bebai
16 Adoniya, Bigivai, Adini,
Adonijah Bigvai Adin
17 Ateri, Hezekiya, Azuri,
Ater Hezekiah Azzur
18 Hodiya, Hasumu, Bezayi
Hodiah Hashum Bezai
19 Harifu, Anatoti, Nebayi,
Hariph Anathoth (Nebai *Q(K)*)
20 Magipiyasi, Mesulamu, Heziri
Magpiash Meshullam Hezir
21 Mesezabeli, Zadoki, Yaduwa
Meshezabel Zadok Jaddua
22 Pelatiya, Hanani, Ananiya,
Pelatiah Hanan Anaiah
23 Hoseya, Hananiya, Hasubu
Hoshea Hananiah Hasshub
24 Halohesi, Piliha, Sobeki,
Hallohesh Pilha Shobek
25 Rehumu, Hasabiya, Maaseya,
Rehum Hashabnah Maaseiah
26 Ahiya, Hanani, Anani,
and Ahiah Hanan Anan
27 Maluki, Harimu ndi Baana.
Malluch Harim Baanah
28 Ife otsalafe, ndiye kuti ansembe, Alevi, alonda a ku Nyumba ya Mulungu, oyimba nyimbo, ogwira ntchito ku Nyumba ya Mulungu, onse amene anadzipatula pakati pa anthu a mitundu ina kuti atsate malamulo a Yehova, pamodzi ndi akazi athu, ana athu ndi onse amene ali ndi nzeru,
and remnant [the] people [the] priest [the] Levi [the] gatekeeper [the] to sing [the] temple servant and all [the] to separate from people [the] land: country/planet to(wards) instruction [the] God woman: wife their son: child their and daughter their all to know to understand
29 tikuphatikana ndi abale athu wolemekezeka, ndipo tikulonjeza molumbira kuti tidzayenda motsata malamulo a Mulungu amene anapereka kudzera mwa Mose mtumiki wa Mulungu. Tilonjeza kumvera ndi kutsata bwino mawu onse, miyambo yonse ndi malangizo onse a Yehova. Yehova atilange ngati sitidzachita zimenezi.
to strengthen: strengthen upon brother: male-relative their great their and to come (in): come in/on/with oath and in/on/with oath to/for to go: walk in/on/with instruction [the] God which to give: give in/on/with hand: by Moses servant/slave [the] God and to/for to keep: obey and to/for to make: do [obj] all commandment LORD lord our and justice: judgement his and statute: decree his
30 “Ife tikulonjeza kuti sitidzapereka ana athu aakazi kuti akwatiwe ndi amuna a mayiko ena kapena kutenga ana awo aakazi kuti akwatiwe ndi ana athu aamuna.
and which not to give: give(marriage) daughter our to/for people [the] land: country/planet and [obj] daughter their not to take: take to/for son: child our
31 “Ngati anthu a mitundu ina abwera ndi zinthu za malonda, monga tirigu, kudzagulitsa pa tsiku la Sabata, sitidzawagula pa tsiku la Sabata kapena pa tsiku lina lililonse loyera. Pa chaka chilichonse cha chisanu ndi chiwiri tidzagoneka munda wosawulima ndipo tidzafafaniza ngongole zonse.
and people [the] land: country/planet [the] to come (in): bring [obj] [the] ware and all grain in/on/with day [the] Sabbath to/for to sell not to take: buy from them in/on/with Sabbath and in/on/with day holiness and to leave [obj] [the] year [the] seventh and interest all hand
32 “Tikulonjezanso molumbira kuti chaka ndi chaka tizipereka magalamu anayi a siliva kuti zithandize ntchito ya ku Nyumba ya Mulungu wathu.
and to stand: appoint upon us commandment to/for to give: give upon us third [the] shekel in/on/with year to/for service: ministry house: temple God our
33 Ndalamayi izithandiza kulipirira buledi wa pa tebulo, chopereka cha chakudya cha nthawi zonse, zopereka zopsereza za nthawi zonse, zopereka za pa tsiku la Sabata, za pachikondwerero cha Mwezi Watsopano, za pa masiku a chikondwerero osankhika, zopereka za zinthu zopatulika, zopereka za nsembe yopepesera machimo a Aisraeli ndi ntchito ina iliyonse ya ku Nyumba ya Mulungu.
to/for food: bread [the] row and offering [the] continually and to/for burnt offering [the] continually [the] Sabbath [the] month: new moon to/for meeting: festival and to/for holiness and to/for sin: sin offering to/for to atone upon Israel and all work house: temple God our
34 “Ife ansembe, Alevi ndi anthu onse, tachita maere kuti tidziwe pamene banja lathu lililonse lidzabweretsa ku nyumba ya Mulungu wathu pa nthawi yoyikika ya chaka zopereka za nkhuni zoyaka pa guwa lansembe la Yehova Mulungu wathu, monga momwe zinalembedwera mʼMalamulo.”
and [the] allotted to fall: allot upon offering [the] tree: wood [the] priest [the] Levi and [the] people to/for to come (in): bring to/for house: temple God our to/for house: household father our to/for time to appoint year in/on/with year to/for to burn: burn upon altar LORD God our like/as to write in/on/with instruction
35 “Tilonjezanso kuti tidzabwera ndi zipatso zoyamba kucha za mʼminda yathu ndi zipatso zoyamba kucha za mtengo uliwonse wa zipatso chaka ndi chaka kuti tidzapereke ku Nyumba ya Mulungu wathu.”
and to/for to come (in): bring [obj] firstfruit land: soil our and firstfruit all fruit all tree year in/on/with year to/for house: temple LORD
36 “Tidzabweranso nawo ku Nyumba ya Mulungu, kwa ansembe amene amatumikira ku Nyumba ya Mulungu ana athu aamuna oyamba kubadwa ndi ana angʼombe oyamba kubadwa monga zalembedwera mu Malamulo. Tidzaperekanso ana oyamba kubadwa a ziweto zathu ndi ana ankhosa oyamba kubadwa.”
and [obj] firstborn son: child our and animal our like/as to write in/on/with instruction and [obj] firstborn cattle our and flock our to/for to come (in): bring to/for house: temple God our to/for priest [the] to minister in/on/with house: temple God our
37 “Ndiponso ku zipinda za Nyumba ya Mulungu wathu, kwa ansembe tidzaperekanso mtanda wathu wa buledi wa ufa ndi mphatso zina monga zipatso za mtengo uliwonse, vinyo ndi mafuta. Tidzaperekanso kwa alevi chakhumi cha mbewu zathu pakuti alevi ndiwo amasonkhanitsa chakhumi mʼmidzi yathu yonse.
and [obj] first: beginning dough our and contribution our and fruit all tree new wine and oil to come (in): bring to/for priest to(wards) chamber house: temple God our and tithe land: soil our to/for Levi and they(masc.) [the] Levi [the] to tithe in/on/with all city service: work our
38 Wansembe, mdzukulu wa Aaroni azikhala pamodzi ndi Alevi pamene akulandira chakhumi. Ndipo Alevi azibwera ndi chakhumicho ku nyumba ya Mulungu wathu, kuzipinda zosungiramo chuma.”
and to be [the] priest son: descendant/people Aaron with [the] Levi in/on/with to tithe [the] Levi and [the] Levi to ascend: establish [obj] tithe [the] tithe to/for house: temple God our to(wards) [the] chamber to/for house: home [the] treasure
39 Choncho Israeli, kuphatikiza zidzukulu za Alevi, azipititsa zopereka za tirigu, vinyo ndi mafuta ku zipinda zosungiramo katundu wopatulika, komanso kokhala ansembe amene akutumikira pamodzi ndi alonda a ku Nyumba ya Mulungu ndi anthu oyimba nyimbo. “Kwambiri ife sitidzaleka kusamala Nyumba ya Mulungu.”
for to(wards) [the] chamber to come (in): bring son: descendant/people Israel and son: descendant/people [the] Levi [obj] contribution [the] grain [the] new wine and [the] oil and there article/utensil [the] sanctuary and [the] priest [the] to minister and [the] gatekeeper and [the] to sing and not to leave: neglect [obj] house: temple God our

< Nehemiya 10 >