< Nahumu 2 >
1 Wodzathira nkhondo akubwera kudzalimbana nawe, Ninive. Tetezani malinga anu, dziyangʼanani ku msewu, konzekerani nkhondo, valani dzilimbe.
Ka raphoe hane tami teh na hmalah a pha toe. Nange rapanim hah ring leih. Na keng hah caksak nateh tha kâ lat leih.
2 Yehova adzabwezeretsa ulemerero wa Yakobo ngati ulemerero wa Israeli, ngakhale anthu owononga anawawononga kotheratu ndipo anawononganso mpesa wawo.
Bangkongtetpawiteh, Cathut teh Isarelnaw e a lentoenae patetlah Jakop e a lentoenae hah ao sak toe. Ka raphoe e taminaw ni Jakop e catoun, a raphoe teh, ahnie a cakang hai koung a raphoe toe.
3 Zishango za ankhondo ake ndi zofiira; asilikali ake avala zovala zofiirira. Zitsulo za pa magaleta zikunyezimira tsiku la kukonzekera kwake. Akuonetsa mikondo ya mkungudza yonoledwa.
Athakaawme taminaw ni ka paling e saiphei a patuep awh teh ka paling e khohna a kho awh. Ranglengnaw hah tahloi hoi laklak a ang teh, tahroenaw teh thouk a kâroe awh.
4 Magaleta akuthamanga mʼmisewu akungothamangathamanga pa mabwalo. Akuoneka ngati miyuni yoyaka; akuthamanga ngati chingʼaningʼani.
Ranglengnaw teh cahucahu kacailah lam dawk atunglah, akalah a yawng awh. Hmaito patetlah a paling teh sumpa patetlah a yawng awh.
5 Iye akuyitanitsa asilikali ake wolemekezeka, koma iwo akubwera napunthwa. Akuthamangira ku linga la mzinda; akuyimika chodzitchinjirizira pamalo pake.
Ransanaw a hroecoe teh ahnimouh ni ayânaw dei a tanawt awh. Khorapan koe karanglah a cei awh teh ramvengnae khu a sak awh.
6 Atsekula zipata zotchinga madzi a mu mtsinje ndipo nyumba yaufumu yagwa.
Tui longkha a kamawng teh siangpahrang im a rawk toe. Nineveh tanglanaw e a khohna a rading pouh teh,
7 Zatsimikizika kuti mzinda utengedwa ndi kupita ku ukapolo. Akapolo aakazi akulira ngati nkhunda ndipo akudziguguda pachifuwa.
bakhu patetlah khui laihoi lungtabue a ratup awh.
8 Ninive ali ngati dziwe, ndipo madzi ake akutayika. Iwo akufuwula kuti, “Imani! Imani!” Koma palibe amene akubwerera.
Ayan hoiyah Nineveh khopui teh tuinawk patetlah doeh ao. Atuteh tui a lawng toe, kangdout awh, kangdout awh telah kahram nakunghai apinihai kamlang sin hoeh.
9 Funkhani siliva! Funkhani golide! Katundu wake ndi wochuluka kwambiri, chuma chochokera pa zinthu zake zamtengowapatali!
Ngun lawm awh. Sui hai lawm awh. Ngai kawi e hnopainaw suitabu thung e rasa teh baw thai hoeh.
10 Iye wawonongedwa, wafunkhidwa ndipo wavulidwa! Mitima yasweka, mawondo akuwombana, anthu akunjenjemera ndipo nkhope zasandulika ndi mantha.
Khopui teh luengpalueng lah ao. Hnopai awm hoeh. Tami kingdi. Khoca pueng teh a lungpout awh, khokpakhu kâkhawng lahoi a keng a pataw awh teh, minhmai ka tamang lah ao awh.
11 Kodi tsopano dzenje la mikango lili kuti, malo amene mikango inkadyetserako ana ake, kumene mkango waumuna ndi waukazi unkapitako, ndipo ana a mkango sankaopa kanthu kalikonse?
Sendek a onae hmuen, sendek a canae hmuen, sendek canaw ni apihai kâtaket sak laipalah a onae hmuen teh na maw ao.
12 Mkango waumuna unkapha nyama yokwanira ana ake ndiponso kuphera nyama mkango waukazi, kudzaza phanga lake ndi zimene wapha ndiponso dzenje lake ndi nyama imene waphayo.
Sendek ni a canaw hanelah a kei teh, a manunaw hanelah a lahuen a kara pouh teh, a kâkhu dawk a kei e moi hoi akawi sak.
13 Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Ine ndikutsutsana nawe. Ndidzatentha magaleta ako mpaka utsi tolotolo, ndipo lupanga lidzapha mikango yako yayingʼono; sindidzakusiyira chilichonse choti udye pa dziko lapansi. Mawu a amithenga anu sadzamvekanso.”
Ransahu BAWIPA ni a dei e teh, nange avanglah ka o han. Nange ranglengnaw hah hmai koung ka sawi han. Na sendeknaw hah tahloi hoi ka thei han. Na lawp e hnonaw talai dawk hoi ka takhoe han. Nange na patounenaw e lawk hah apinihai bout thai mahoeh toe.