< Mika 5 >
1 Iwe mzinda wa anthu ankhondo, sonkhanitsa anthu ako ankhondo, pakuti anthu atizungulira kuti alimbane nafe. Adzakantha ndi ndodo pa chibwano cha wolamulira wa Israeli.
І згрома́джуйсь тепер, дочко то́впищ! Обло́гу вчинили на нас, трости́ною б'ють по щоці Ізраїлевого суддю́...
2 “Koma iwe Betelehemu Efurata, ngakhale uli wonyozeka pakati pa mafuko a Yuda, mwa iwe mudzatuluka munthu amene adzalamulira Israeli, amene chiyambi chake nʼchakalekale, nʼchamasiku amakedzana.”
А ти, Віфлеєме-Єфра́те, хоч малий ти у тисячах Юди, — із тебе Мені ви́йде Той, що бу́де Владика в Ізраїлі, і відда́вна поста́ння Його, від днів вікові́чних.
3 Nʼchifukwa chake Israeli adzasiyidwa mpaka pa nthawi imene mayi amene ali woyembekezera adzachire. Ndipo abale ake onse otsalira adzabwerera kudzakhala pamodzi ndi Aisraeli.
Тому́ Він їх видасть до ча́су, аж поки ота не породить, що має родити, а останок братів Його ве́рнеться до Ізраїлевих синів.
4 Iye adzalimbika, ndipo adzaweta nkhosa zake mwa mphamvu ya Yehova, mu ulemerero wa dzina la Yehova Mulungu wake. Ndipo iwo adzakhala mu mtendere, pakuti ukulu wake udzakhala ponseponse pa dziko lapansi.
І стане, і буде Він па́сти Господньою силою, вели́чністю Йме́ння Господа Бога Свого́. І осядуть вони, бо Він стане великий тепер аж до кі́нців землі!
5 Ndipo Iye adzakhala mtendere wawo. Asiriya akadzalowa mʼdziko lathu ndi kuyamba kuthira nkhondo malo athu otetezedwa, tidzawadzutsira abusa asanu ndi awiri, ngakhalenso atsogoleri asanu ndi atatu.
І Він буде миром. Як при́йде до нашого краю Ашшу́р, і буде топта́тись по наших пала́тах, то поставимо на нього сім па́стирів та во́сьмеро лю́дських княжа́т.
6 Iwo adzagonjetsa dziko la Asiriya ndi lupanga, dziko la Nimurodi adzalilamulira mwankhondo. Adzatipulumutsa kwa Asiriya akadzafika mʼmalire a mʼdziko lathu kudzatithira nkhondo.
І вони будуть па́сти мечем край Ашшу́ра, край же Німро́да — у воро́тях його. Та Він від Ашшу́ра врятує, як той при́йде в наш край, і коли буде топтатись по наших грани́цях.
7 Otsalira a Yakobo adzakhala pakati pa mitundu yambiri ya anthu ngati mame ochokera kwa Yehova, ngati mvumbi pa udzu, omwe sulamulidwa ndi munthu kapena kudikira lamulo la anthu.
І Яковів за́лишок буде посе́ред числе́нних наро́дів, як роса та від Господа, як той дощ на траві, і він наді́ї не кла́стиме на чоловіка, і не буде наді́ї склада́ти на лю́дських синів.
8 Otsala a Yakobo adzakhala pakati pa mitundu ya anthu, mʼgulu la anthu a mitundu yambiri, ngati mkango pakati pa nyama za mʼnkhalango. Ngati mwana wa mkango pakati pa gulu la nkhosa, amene pozidutsa amazidya ndi kuzikhadzula, ndipo palibe angathe kuzilanditsa.
І Яковів за́лишок буде між лю́дами, серед числе́нних наро́дів, як лев між лісно́ю худо́бою, як левчу́к між ота́рами ове́ць, — що як він перехо́дить, то то́пче й шматує, і немає ніко́го, хто б зміг урятувати.
9 Mudzagonjetsa adani anu, ndipo adani anu onse adzawonongeka.
Хай зведе́ться рука твоя на твоїх ненави́сників, і хай всі вороги твої ви́тяті бу́дуть!
10 Yehova akuti, “Tsiku limenelo ndidzawononga akavalo anu onse ndi kuphwasula magaleta anu.
І станеться в день той, говорить Госпо́дь, — і ви́тну Я ко́ні твої з-серед тебе, і колесни́ці твої повигу́люю.
11 Ndidzawononga mizinda ya mʼdziko mwanu ndi kugwetsa malinga anu onse.
І пони́щу міста́ твого кра́ю, і всі тверди́ні твої порозвалюю.
12 Ndidzawononga ufiti wanu ndipo sikudzakhalanso anthu owombeza mawula.
І повипо́люю ча́ри з твоєї руки, і ворожби́тів у тебе не бу́де.
13 Ndidzawononga mafano anu osema pamodzi ndi miyala yanu yopatulika imene ili pakati panu; simudzagwadiranso zinthu zopanga ndi manja anu.
І понищу бовва́ни твої та жерто́вні стовпи́ твої з-посеред тебе, і ти чи́нові рук своїх більше не бу́деш вклоня́тися.
14 Ndidzazula mitengo ya mafano a Asera imene ili pakati panu, ndipo ndidzawononga mizinda yanu.
І повитина́ю дере́ва жерто́вні твої з-серед тебе, і міста́ твої вигублю.
15 Ndidzayilanga mwaukali ndi mokwiya mitundu imene sinandimvere Ine.”
І в гніві та в лютості по́мсту вчиню́ над наро́дами, що Мене не послу́хались!