< Mika 3 >

1 Ndipo ine ndinati, “Tamverani, inu atsogoleri a Yakobo, inu olamulira nyumba ya Israeli. Kodi sindinu oyenera kudziwa kuweruza molungama,
Dilia! Isala: ili ouligisu dunu! Nabima! Dilia da moloidafa hou noga: le ouligimu galu!
2 inu amene mumadana ndi zabwino ndi kukonda zoyipa; inu amene mumasenda khungu la anthu anga, ndipo mumakungunula mnofu pa mafupa awo;
Be dilia da noga: idafa hou higale, wadela: i hou hanasa. Dilia da na fi dunu amo esasulumuna: wane gadofo houga: le, hu gaga: ne fasisa.
3 inu amene mumadya anthu anga, mumasenda khungu lawo ndi kuphwanya mafupa awo; inu amene mumawadula nthulinthuli ngati nyama yokaphika?”
Dilia da na fi na dagosa! Dilia da ilia gadofo houga: le, ilia gasa fifili, amola ilia da: i hodo hu gobele nasu defele hedesisa.
4 Pamenepo adzalira kwa Yehova, koma Iye sadzawayankha. Nthawi imeneyo Iye adzawabisira nkhope yake chifukwa cha zoyipa zimene anazichita.
Esoha da mana, amo doaga: sea, dilia da Hina Godema dini imunu. Be Eda dilima dabe hame adole imunu. Dilia da wadela: le hamoiba: le, E da dilia sia: ne gadobe hame nabimu.
5 Yehova akuti, “Aneneri amene amasocheretsa anthu anga, ngati munthu wina awapatsa chakudya amamufunira ‘mtendere;’ ngati munthu wina sawapatsa zakudya amamulosera zoyipa.
Balofede dunu ilia Na fi dunuma ogogole olelesa. Amo balofede dunu da nowa ilima bidi iasea, ilima hahawane olofosu ilegele ba: la la. Be nowa da ilima bidi hame iasea, ilima wadela: i gegesu fawane ilegele ba: la la. Hina Gode da amo balofede dunuma amane sia: sa.
6 Nʼchifukwa chake kudzakuderani, simudzaonanso masomphenya, mdima udzakugwerani ndipo simudzawombezanso. Dzuwa lidzawalowera aneneriwo, ndipo mdima udzawagwera.
“Balofede dunu dilia! Dilia eso da dagomu gadenesa! Dilia eso da wali dagomu galebe. Dilia da bu ba: lalumu da hamedei ba: mu. Bai dilia da Na fi dunuma ogogoi. Amola dilia da fa: no misunu liligi da hame ba: lalumu.
7 Alosi adzachita manyazi ndipo owombeza mawula adzanyazitsidwa. Onse adzaphimba nkhope zawo chifukwa Mulungu sakuwayankha.”
Amo fa: no misunu hou ba: la: lusu dunu ilia da fa: no misunu hou hame ba: beba: le, gogosiamu. Gode da ilima dabe hame adole imunuba: le, ilia da dunu mimogoa gogosiasu ba: mu.
8 Koma kunena za ine, ndadzazidwa ndi mphamvu, ndi Mzimu wa Yehova, ndi kulungama, ndi kulimba mtima, kuti ndilalikire za kugalukira kwa Yakobo, kwa Israeli za tchimo lake.
Be nama da Hina Gode da Ea gasa bagade A: silibuga nama nabalesisa. E da nama moloidafa asigi dawa: su amola dogo denesini dawa: su iaha. Amaiba: le, na da Isala: ili dunu ilima ilia wadela: i hou diliwaneya udidimusa: dawa:
9 Imvani izi, inu atsogoleri a nyumba ya Yakobo, inu olamulira nyumba ya Israeli, inu amene mumadana ndi kuweruza kolungama; ndipo mumakhotetsa zinthu zonse zolondola;
Isala: ili ouligisu hina dunu, dilia! Na sia: nabima! Dilia da moloidafa hou higabeba: le, wadela: i hou fawane hamomusa: bagade hanasa.
10 inu amene mukumanga Ziyoni pokhetsa magazi, ndi Yerusalemu ndi kuyipa kwanu.
Fedege agoane, dilia Yelusaleme moilai bai bagade gagusia, fane legesu amola moloi hou hame amoga bai fa: le gagusa.
11 Atsogoleri ake amalandira chiphuphu kuti aweruze, ansembe ake amalandira malipiro kuti alalikire, ndipo aneneri ake amanenera kuti alandire ndalama. Komatu amatsamira pa Yehova nʼkumanena kuti, “Kodi Yehova sali pakati pathu? Palibe tsoka limene lidzatigwere.”
Moilai bai bagade ouligisu dunu ilia da hano suligisu hawa: fawane hamosa. Gobele salasu dunu da bidi lamusa: fawane Sema olelesa. Balofede dunu ilia da bidi lamusa: fawane, fa: no misunu hou olelesa. Be ilia huluane da Hina Gode da ilima esala amane sia: sa. Ilia da amane sia: sa, “Hina Gode da ninima esalebeba: le, ninima se nabasu da hame doaga: mu!”
12 Choncho chifukwa cha inu, Ziyoni adzatipulidwa ngati munda, Yerusalemu adzasanduka bwinja, ndipo phiri la Nyumba ya Mulungu lidzasanduka nkhalango yowirira.
Amaiba: le, dilia da bai hamobeba: le, Saione moilai bai bagade da osobo gidinasuga dogoi agoai ba: mu. Yelusaleme moilai bai bagade da mugululi lelegela heda: i dialebe ba: mu. Amola Debolo agolo da iwila hamoi dagoi ba: mu.

< Mika 3 >