< Mateyu 9 >

1 Yesu analowa mʼbwato nawoloka, ndipo anabwera ku mudzi wa kwawo.
U Yesu ahinjila mwitoli, ahafwimila ahafiha hunsi ya hakhalaga.
2 Amuna ena anabwera ndi munthu wakufa ziwalo kwa Iye atamugoneka pa mphasa. Yesu ataona chikhulupiriro chawo anati kwa wakufa ziwaloyo, “Limba mtima mwana wanga, machimo ako akhululukidwa.”
Bhahanetela, umuntu ya polile ubili agonile pashitala. Lwahahulola ulwitiho lwabho u Yesu ahamuzya umuntu yapolile, “Mwanawi ushanje, ukhombhosheye imbibhi zyaho.”
3 Pamenepo aphunzitsi ena amalamulo anaganiza mu mtima mwawo kuti, “Munthu uyu akuchitira Mulungu mwano.”
Abhalimu bhamo abhilenga bhahayanjizanya bhibho hu bhibho, “Umuntu unu alinindigo”
4 Ndipo podziwa maganizo awo Yesu anati, “Bwanji mukuganiza zoyipa mʼmitima mwanu?
U Yesu ahamanya insibho zyabho naje yeenu musibha imbibhi mumyoyo ginyu?
5 Chapafupi ndi chiti kunena kuti, ‘Machimo ako akhululukidwa’ kapena kunena kuti, ‘Imirira ndipo yenda?’
Henu hehinza aje ikhobhosheye, 'Imbibhi zyaho na aje, 'imililila ujende?'
6 Tsono kuti mudziwe kuti Mwana wa Munthu ali ndi ulamuliro pa dziko wokhululuka machimo, pamenepo anati kwa wakufa ziwaloyo, ‘Imirira, tenga mphasa yako kazipita kwanu.’”
Ishi mumanye aje wa Adamu alini nguvu izyahubhakhobhoshele imbibhi.” ahayanjile izi hwula yapolile, “Imilila, uyitwinshe igodoro lyaho ubhale hukhaya yaho”
7 Ndipo munthuyo anayimirira napita kwawo.
Umuntu ula ahimilila nasogole abhale hukhaya yakwe.
8 Gulu la anthu litaona izi, linadzazidwa ndi mantha ndipo linalemekeza Mulungu amene anapereka ulamuliro kwa anthu.
Impuga ya bhantu lwe bhahalola igo, bhahaswijile na huntime u Ngulubhi, yabhapiye inguvu izyo abhantu.
9 Ndipo Yesu atachoka kumeneko, anaona munthu wina dzina lake Mateyu, atakhala mʼnyumba ya msonkho. Anati kwa iye, “Nditsate Ine.” Ndipo iye ananyamuka namutsata.
U Yesu lwahashilaga afume ipo ahanola umuntu yahwitwa itawa Mathayo, yahakhiye pebhafumizya insoho. Wope ahabhabhuzya, “Munfuate ani” Wope ahimilila ahafwata.
10 Ndipo pamene Iye ankadya mʼnyumba, onani, amisonkho ndi ochimwa ambiri anabwera nakhala pansi pamodzi ndi Yesu ndi ophunzira ake.
U Yesu lwahakhiye alye ishalye munyumba, bhahinzi bhebhafumya insoho bhabhinji na bhantu abhimbibhi bhahaliye peka ishalye nu Yesu peka abhasunde bhakwe.
11 Ndipo Afarisi poona izi, anati kwa ophunzira ake, “Nʼchifukwa chiyani Aphunzitsi anu akudya pamodzi ndi amisonkho ndi ochimwa?”
Afalisayo lwe bhahalola isho bhahabhabhuzya abhasende bhakwe, yeenu u Yesu alya ishalye na bhantu abhafumya insoho na bhantu abhimbibhi?”
12 Yesu atamva, anati, “Munthu wamoyo safuna singʼanga ayi, koma wodwala.
U Yesu lwa ahivwa igo, wope ahayanga “Abhantu bhesebhabhinile sebhahwanza unganga, ila bhebhabhinile.
13 Koma pitani kaphunzireni tanthauzo la mawu awa: ‘Ndimafuna chifundo osati nsembe ayi.’ Pakuti sindinabwere kudzayitana olungama koma ochimwa.”
Ihwanziwa huje mubhale mumanyile imaana yakwe, “Insungwa irehema siga izabihu” Pipo senahinzile hubhantu abhimbibhi.
14 Ndipo ophunzira a Yohane anabwera namufunsa Iye kuti, “Bwanji ife ndi Afarisi timasala kudya koma ophunzira anu sasala kudya?”
Abhasunde bha Yohana bhahinza hukwakwe na aje, “Yeenu ati na mafalisayo tifunga, lakini abhasunde bhaho sebhafunga?”
15 Yesu anayankha kuti, “Kodi oyitanidwa ku ukwati angamalire bwanji pamene mkwati ali naye pamodzi? Nthawi idzafika pamene mkwatiyo adzachotsedwa ndi pamene adzasala kudya.”
U Yesu ahabhabhuzya ahaga, Je abhalolezi bhi weji bhangaswimalwe bhali peka nu gosi wiweji? Lakini insiku zihwinza insiku ugosi wi weji ahayisogola pebhahayifunga.
16 Ndipo palibe munthu amasokerera chigamba chatsopano pa chovala chakale chifukwa chigambacho chidzachoka ndipo chibowocho chidzakula kuposa kale.
Nuumo umuntu yabhiha ishipande shimwenda umpya humwenda uwimandi, ishulaka shibhadebushe afume humwenda na abazushe haani hubhafumile.
17 Kapena sathira vinyo watsopano mʼmatumba akale; akatero, matumba akalewo adzaphulika ndipo vinyoyo adzatayika, matumbawo adzawonongeka; satero ayi. Amathira vinyo watsopano mʼmatumba atsopanonso ndipo zonse zimasungika.
Nabhamo abhantu bhebhabhiha ihombwa mushombo ishihombwa inkuulu, nkushele bhabhomba, ingozi ibhadebushe ihambwa ibhafume na nanjishe. Badala yakwe, ubhiha ihombwa impya mungozi impya vyonti vibhabha salama.
18 Pamene ankanena zimenezi, mkulu wa sunagoge anabwera namugwadira Iye nati, “Mwana wanga wamkazi wamwalira posachedwapa koma tiyeni mukasanjike dzanja lanu pa iye ndipo adzakhala ndi moyo.”
U Yesu lwahabhabhuzya amambo iga, ahali, ugosi umo ahamwinamila mwilongolela lyakwe ahaga, “Unindu wani afwiye shinishi inza umponye abhapone abhabhe mwoomi.
19 Yesu ndi ophunzira ake ananyamuka napita naye pamodzi.
U Yesu ahimilila na huusojelele na bhasunde bhakwe.
20 Panali mayi wina amene ankadwala nthenda yotaya magazi kwa zaka khumi ndi ziwiri ndipo anadza mʼmbuyo mwake nakhudza mkanjo wake.
Ahali, ushi yahafumaga idanda amaha kumi na mbili ahasojelela pipi nu Yesu ahayikhata inkanzu ya Yesu.
21 Iyeyo anati mwa iye yekha, “Nditangokhudza kasonga ka mkanjo wake, ine ndidzachiritsidwa.”
Pipo ahayile, “Nkushele na bhukhata umweudo wa Yesu imbapone.”
22 Ndipo Yesu anatembenuka namuona mayiyo nati, “Limbani mtima mayi iwe, chikhulupiriro chako chakuchiritsa.” Nthawi yomweyo mayiyo anachiritsidwa.
U Yesu ahagaluhana na humwenye na humuuzye, “Ninda uyipele umwoyo, nu ulwitiho lwaho lubhombile aje upone,” Ahabhalilizyo hiniho unshi ula ahapona.
23 Yesu atalowa mʼnyumba ya mkulu wa sunagoge ndi kuona oyimba zitoliro ndi gulu la anthu ochita phokoso,
U Yesu lwahafiha hukhaya ya gosi, ahabhalola bhebhakhoma ifilimbi na impuga ya bhantu yahakhomaga ahalanga.
24 anati, “Tulukani, mtsikanayu sanafe koma ali mtulo.” Koma anamuseka Iye.
Wope ahaga, “Epi ipa, unindu saafwiye agonile. Lelo abheene bhahanseshile haani.
25 Atangowatulutsa anthuwo, analowa mʼnyumba ndipo anagwira dzanja la mtsikanayo ndipo anauka.
Abhantu bhala lwebha fuma hunzi, wope ahinjila huhati na hunkhate inyobhe unindu ahadamuna.
26 Mbiriyi inamveka mʼdera lonse.
Inongwa zyahayeha insi yonti.
27 Yesu atapitirira ulendo wake, amuna awiri osaona anamutsatira Iye, akufuwula kuti, “Tichitireni chifundo, Mwana wa Davide!”
U Yesu lwahashilaga afume pala, abhalume bhabhili bhesebhahwenya amaso bhahausejelela. Bhahendeliye akhole bhahaga, “Tilabha utiponye, Mwana wa Daudi.”
28 Atalowa mʼnyumba, amuna awiri osaonawo anabwera kwa Iye ndipo anawafunsa kuti, “Kodi mukhulupirira kuti ndikhoza kukuchiritsani?” Iwo anayankha kuti, “Inde Ambuye.”
U Yesu lwahafishile hukhaya, bhala bhesabhahwenya amaso bhahinza hukwake. U Yesu ahabhabhuzya, “Muhwitiha huje ingabhaponya?” Bhope bhahaga “Ena, Gosi”
29 Pomwepo anakhudza maso awo nati, “Zichitike kwa inu monga mwachikhulupiriro chanu.”
U Yesu ahakhata amaso gabho naje zibhombeshe isho hulimwe ndeshe ulitiho lwinyu sheluhi”
30 Ndipo anayamba kuona. Yesu anawachenjeza kwambiri nati, “Onani, wina aliyense asadziwe za zimenezi.”
Na amaso gabho gahanda ahwenye. Pe Yesu ahakhajilizya hunguvu na yanje “Mwenyaje umuntu wowonti asahamanye ijambo ili.”
31 Koma iwo anatuluka mʼnyumbamo nafalitsa za Iye mʼchigawo chonse.
Lelo abhantu bhabhili bhahasogoye alumbilile ahusu amambo iga isehemu zyonti izyinkhaya.
32 Pamene iwo ankatuluka kunja, anthu anabwera kwa Iye ndi munthu wogwidwa ndi mzimu wosayankhula.
Pe pinipo abhalume bhala bhabhili lwe bhahasogolaga, ahali, umuntu umo aliyububu impepo zyahamwinjiye bhahaletwa hwa Yesu.
33 Ndipo atatulutsa mzimuwo, munthuyo anayankhula. Gulu la anthuwo linadabwa ndipo linati, “Zinthu zotere sizinaonekepo mu Israeli.”
Impepo lwezyahamwepa umuntu ububu ahanda ayanje. Impuga yahaswiga naje setilolile nkalumo amambo iga gegafumiye mu Israeli.
34 Koma Afarisi anati, “Akutulutsa mizimu yoyipa ndi mphamvu ya mkulu wa ziwanda.”
Lelo afalisayo bhayangaga hwa gosi wi impepo ahugabhinga amapepo.”
35 Yesu anayendayenda mʼmizinda yonse ndi mʼmidzi, kuphunzitsa mʼmasunagoge awo, nalalikira Uthenga Wabwino wa ufumu ndi kuchiritsa nthenda zawo zonse ndi zofowoka za mʼmatupi mwawo.
U Yesu ahabhalile ikhaya zyonti ni vijiji vyonti. Ahendeliye amanyizye mumasinagogi, alumbilile izwi ilyibhumwene na ponye impungo zyonti nu bhuzaifu wonti.
36 Ataona maguluwo, anagwidwa ndi chisoni chifukwa anali ozunzika ndi osowa chithandizo ngati nkhosa zopanda mʼbusa.
Lwa ahenya impuga, ahabhaloleye inkumbu, pipo bhahayimbile navunzishe mumwoyo. Bhahali ndeshi ingole zyesazili nu udimi.
37 Pamenepo anati kwa ophunzira ake, “Zokolola ndi zambiri koma antchito ndi ochepa.
Wope ahabhabhuzya abhasunde bhakwe ahaga, “Amavuno minji, abhabhomba mbombo bhadodo.
38 Nʼchifukwa chake, pemphani Ambuye mwini zokolola kuti atumize antchito ku munda wake.”
Ishi lubhilo tinabhe ugosi wi mavuno, nke huje atume abhabhomba mbombo mugunda gwakwe.”

< Mateyu 9 >