< Mateyu 3 >

1 Mʼmasiku amenewo, Yohane Mʼbatizi anadza nalalikira mʼchipululu cha Yudeya
I mahiku ayo u Yohana Mbatizaji auzile akazetanantya ulukani mumbuga ang'wa Yuda akazelunga,
2 kuti, “Tembenukani mtima chifukwa ufumu wakumwamba wayandikira.”
Leki imilandu kunsoko utemi wa kigulu ukole pakupe.”
3 Uyu ndi amene mneneri Yesaya ananena za iye kuti, “Mawu a wofuwula mʼchipululu, ‘Konzani njira ya Ambuye, wongolani njira zake.’”
Kunsoko yuyu nauligitigwe numunyakidagu u Isaya ikalunga, “Luli la muntu nukitanga mumbuga, leki uza inzila ya Mkulu, gooli kisa imapanda akwe.”
4 Zovala za Yohane zinali zopangidwa ndi ubweya wa ngamira, ndipo amamangira lamba wachikopa mʼchiwuno mwake. Chakudya chake chinali dzombe ndi uchi wa kuthengo.
U Yohana autugae mauli angamia hangi akitunga numusipi wa ndili mkileno kakwe indya yakwe ai ngaga nu uki wa mihaka.
5 Anthu ankapita kwa iye kuchokera ku Yerusalemu ndi ku Yudeya konse ndi ku madera onse a Yorodani.
Hangi Yerusalemu, Yuda ihi, nikisali kihi nikepilimiye umongo wa Yorodani ikalongola kitalakwe.
6 Ndipo akavomereza machimo awo ankabatizidwa mu mtsinje wa Yorodani.
Aizabadisigwa mumongo wa Yorodani nukila itunu imilandu ao.
7 Koma iye ataona Afarisi ndi Asaduki ambiri akubwera kumene ankabatiza, anawawuza kuti, “Ana a njoka inu! Ndani anakuchenjezani kuthawa mkwiyo umene ukubwera?
Sunga akatyatwa unuduu wa mafarisayo ni masadukayo kuza kubadisigwa, akaeela, unye wileli wa nzoka nikete sumu nyenyu numuhuguye kuutiga uubi nupembilye?
8 Onetsani chipatso cha kutembenuka mtima.
Tugi imaintu nahegekile mumilandu, namuloeye Itunda.
9 Ndipo musaganize ndi kunena mwa inu nokha kuti, ‘Tili nawo abambo athu Abrahamu.’ Ndinena kwa inu kuti Mulungu akhoza kusandutsa miyala iyi kukhala ana a Abrahamu.
Leki kusige nukikolya kung'wanyu kutite u Ibrahimu anga tata witu, inge kumuila Itunda uhumile kumuukilya u Ibrahimu iana kupumila mumagwe aya.
10 Tikukamba pano nkhwangwa yayikidwa kale pa mizu ya mitengo, ndipo mtengo umene subala chipatso chabwino udulidwa ndi kuponyedwa pa moto.
Ihengo aikwa mumuli wa muti, kulule umuti nishawipeza indya ninza witeng'wa nukugung'wa mumoto.
11 “Ine ndikubatizani ndi madzi kusonyeza kutembenuka mtima. Koma pambuyo panga akubwera wina amene ali ndi mphamvu kuposa ine, amene sindiyenera kunyamula nsapato zake. Iyeyu adzakubatizani ndi Mzimu Woyera ndi moto.
Kumubadiza kunzila amazi, nukumuhugilya muhueli. Kululo uyu nupembilye ukete ingulu kukila unene, hangi kuleng'wa lukulu kukenka ilatu yakwe. Nuanso ukuabadisa kukeela ng'waung'welu nu moto.
12 Mʼdzanja lake muli chopetera ndipo adzayeretsa popunthirapo pake nadzathira tirigu wake mʼnkhokwe ndi kutentha zotsalira zonse ndi moto wosazima.”
Ipetelo nilakupelela ingano likole mumikono akwe, kilingila iyo ninza misalanka. Kululo gwa iyo nikite ipuko ikusonswa umoto uo nishawilima.
13 Pamenepo Yesu anabwera kuchokera ku Galileya kudzabatizidwa ndi Yohane mu mtsinje wa Yorodani.
Sunga u Yesu akaza kupembelya kugalilaya akapika mumongo wa Yorodani akabadisigwa nu Yohana.
14 Koma Yohane anayesetsa kumukanira nati, “Ndiyenera kubatizidwa ndi Inu, bwanji Inu mubwera kwa ine?”
Yohana akahia amugilye akalunga, unene ntakile mbadisigwe nuewe, nikawaza kitalane?
15 Yesu anayankha kuti, “Zibatero tsopano, ndi koyenera kwa ife kuchita zimenezi kukwaniritsa chilungamo chonse.” Ndipo Yohane anavomera.
U Yesu akasusha akalunga, “Gomba itule uu itungile. Kunsoko yatula kukondanilye itai ehi.” Sunga u Yohana akamugombya.
16 Yesu atangobatizidwa, nthawi yomweyo potuluka mʼmadzi, kumwamba kunatsekuka ndipo taonani, Mzimu wa Mulungu anatsika ngati nkhunda natera pa Iye.
Naiwamala kubadisigwa, u Yesu akapuma mumazi, Ilunde likaluguka kitalakwe. Akamuona ng'waung'welu wang'wi Tunda akazesima anga inkunda nukukilaja migulya akwe.
17 Ndipo mawu anamveka kuchokera kumwamba kuti, “Uyu ndiye mwana wanga wokondedwa amene ndikondwera naye.”
Goza, luli ailupumie kilunde lukalunga, “Uyu ng'waane mlowa. ni ndoeigwe nangulu nung'wenso.”

< Mateyu 3 >