< Mateyu 27 >
1 Mmamawa, akulu a ansembe onse ndi akuluakulu anavomerezana kuti aphe Yesu.
Pabaikite kindae, akolo bote ba Makuhani ni apindo ba bandu babile ni njama kwaajili ya Yesu linga bamulage.
2 Anamumanga, napita naye kukamupereka kwa bwanamkubwa Pilato.
Batikuntaba, batikunongoya, na kumwikiya kwa liwali Pirato.
3 Yudasi, amene anamupereka Iye, ataona kuti Yesu waweruzidwa kuti akaphedwe, anatsutsika mu mtima mwake nakabweza ndalama zamasiliva makumi atatu zija kwa akulu a ansembe ndi kwa akuluakulu.
Boka po wakati Yuda, ywabile atikunsaliti, amweni panga Yesu bayomwile kumwukumu, atijuta no kelebuya ipande thelathini ya mbanje kwa akolo ba makuhani na apindo,
4 Iye anati, “Ndachimwa pakuti ndapereka munthu wosalakwa.” Iwo anayankha nati, “Ife tilibe nazo kanthu izo ndi zako.”
no baya, “Nipangite sambi kwa kwisaliti mwai yange makosa.” Ngaban'yangwa, “Twena ituhusu namani? ugalinge ago wa mwene.”
5 Pamenepo Yudasi anaponya ndalamazo mʼNyumba ya Mulungu nachoka. Kenaka anapita nakadzimangirira.
Boka po kaitakulya pae yelo ipande thelathini ya mbanje muhekalu, kabuka kachake kwikongela mwene.
6 Akulu a ansembe anatola ndalamazo nati, “Sikololedwa ndi lamulo kuti ndalamazi tiziyike mosungira chuma cha Mulungu, popeza ndi ndalama za magazi.”
Nkolo wa Makuhani atikuitola yelo ipande thelathini ya mbanje no baya, “Halali kwaa kwibeka mbanje yeno mu'hazina, mana yabile garama ya mwai.”
7 Choncho anagwirizana kuti ndalamazo azigwiritse ntchito pogulira munda wa wowumba mbiya kuti ukhale manda alendo.
Batikujadilyana kwa pamope batikwitola yelo ipande thelathini ya mbanje batumi kupema mgunda wosikiya ageni.
8 Ndi chifukwa chake umatchedwa munda wamagazi mpaka lero lino.
Kwasababu yelo mgunda woo walowa kemelwa, “Mgunda wa mwai” mpaka leno.
9 Pamenepo zimene anayankhula mneneri Yeremiya zinakwaniritsidwa kuti, “Anatenga ndalama zamasiliva makumi atatu mtengo umene anamuyikira Iye anthu a Israeli.
Linga lelo likowe lyaalongei nabii Yeremia latimii, kabaya, “Batwelile ipande thelathini ya mbanje, garama yaipangilwe ni bandu ba Israel kwaajili yake,
10 Ndipo anazigwiritsa ntchito kugula munda wa wowumba mbiya monga mmene Ambuye anandilamulira ine.”
ni baatumi kwa mgunda wa mfinyanzi, kati Ngwana mwaanibakiye.”
11 Pa nthawi yomweyo Yesu anayimirira pamaso pa bwanamkubwa ndipo bwanamkubwayo anamufunsa Iye kuti, “Kodi ndiwe Mfumu ya Ayuda?” Koma Yesu anayankha kuti, “Mwanena ndinu.”
Nga Yesu ban'yemike nnonge ya liwali, na liwali atikunaluya, “Wenga wa mpwalume wa Ayahudi?” Yesu kayangwa, “Wenga wabaya nyoo.”
12 Pamene akulu a ansembe ndi akuluakulu ankamuneneza, sanayankhe kanthu.
Lakini pabansitaki akolo ba Makuhanini apindo, ayangwi kwaa kilebe chochote.
13 Kenaka Pilato anamufunsa Iye kuti, “Kodi sukumva zinthu zimene akukunenerazi?”
Boka po Pilato kammakiya, “Uyowine kwaa masitaka goti kunani yako?
14 Koma Yesu sanayankhe ngakhale mawu amodzi mpaka bwanamkubwa anadabwa kwambiri.
Lakini anyangwi kwaa hata likowe limo, liwali atisangala muno.
15 Pa nthawiyi chinali chizolowezi cha bwanamkubwa kuti pachikondwerero cha Paska amamasula wamʼndende wosankhidwa ndi anthu.
Yabile mu'sikukuu kati yabile desturi ya liwali kunyogolya mtabilwe yumo ywabachalwa no kipenga sa bandu.
16 Pa nthawiyo anali ndi wamʼndende woyipa kwambiri dzina lake Baraba.
Muda woo abile mtabilwa sugu lina lyake Baraba.
17 Gulu la anthu litasonkhana, Pilato anawafunsa kuti, “Ndi ndani amene mufuna kuti ndikumasulireni; Baraba kapena Yesu wotchedwa Khristu?”
Tubwe pabakwembine pamope, Pilato atikwalaluya, Nyai ywamupala ninyogoli kwa hiyali yinu?”Baraba au Yesu ywaikema Kristo.
18 Pakuti anadziwa kuti anamupereka Yesu chifukwa cha kaduka.
Kwa mana atangite panga bammoywe kwa kunchukya.
19 Pamene Pilato anakhala pa mpando woweruza, mkazi wake anamutumizira uthenga uwu, “Musachite kanthu ndi munthuyo, ndi wosalakwa pakuti ndavutika kwambiri lero mʼmaloto chifukwa cha munthuyo.”
Patami pakitego chake cha hukumu, nyumbowe atumite neno kabaya, “Kana upange likowe lyolyote kwa mundu ywange hatia. Mana nititeseka muno mundoto ya leno kwa mwanja ywembe.”
20 Koma akulu a ansembe ndi akuluakulu ananyengerera gulu la anthu kuti apemphe Baraba ndi kuti Yesu aphedwe.
Tumbwe akolo ba Makuhani ni apindo, batikwakingindwa bandu bannobe Baraba, na Yesu bamulage.
21 Bwanamkubwayo anafunsa kuti, “Ndi ndani mwa awiriwa amene mufuna ine ndikumasulireni?” Iwo anayankha kuti, “Baraba.”
Liwali atikwalaluya, “Kati ya haba abele ywako nin'yogolii?” Ngababaya, “Baraba.”
22 Pilato anafunsa kuti, “Nanga ndichite chiyani ndi Yesu wotchedwa Khristu?” Onse anayankha kuti “Mpachikeni!”
Pilato kaabakiya nipange kele kwa Yesu ywakemelwa Kristo?” Bote kabanyangwa, “Anyongelwe.”
23 Pilato anafunsa kuti, “Chifukwa chiyani? Wachita choyipa chotani?” Koma anachita phokoso nafuwula kwambiri kuti, “Mpachikeni!”
Ni ywembe kabaya, “mwanja namani, kosa gani lyaapangite?”Ngabatondobiye lilobe kabakemelya, “Anyongolwe.”
24 Pilato ataona kuti samaphulapo kanthu, koma mʼmalo mwake chiwawa chimayambika, anatenga madzi nasamba mʼmanja mwake pamaso pa gulu la anthu. Iye anati “Ine ndilibe chifukwa ndi magazi a munthu uyu, ndipo uwu ndi udindo wanu!”
Kwa eyo wakati Pilato paibweni aweza kwaa panga kikowe chochote, ila furugu yende tumba, atweti mache auluwi maboko gake noge yabe, no baya, “Nenga ntopo atiya kwa mundu yoo ywange likosa. Mugalinge gaa mwabene.”
25 Anthu onse anayankha nati, “Magazi ake akhale pa ife ndi pa ana athu!”
Bandu bote kababaya, “Mwai yake ibe kun ani yitu na bana bitu.”
26 Pamenepo anawamasulira Baraba koma analamula kuti Yesu akakwapulidwe, ndipo anamupereka kuti akapachikidwe.
Boka po anyogoli Baraba kasabe, lakini akombwi ni mjeredi Yesu atikwapeya kwabe bayende kusulubilwa.
27 Pamenepo asilikali abwanamkubwayo anamutenga nalowa naye ku bwalo la milandu ndipo anasonkhanitsa gulu lonse la asilikali namuzungulira Iye.
Ni askari ba liwali kabantola Yesu mpaka Praitorio na likundi lya maaskari bote batikusanyika.
28 Anamuvula malaya ake namuveka Iye malaya ofiira aufumu.
Kabamwulike ngobo yake na kungwalika likanju lya rangi ngele.
29 Ndipo kenaka analuka chipewa chaminga nachiyika pa mutu pake. Anamugwiritsa ndodo mʼdzanja lake lamanja nagwada pamaso pake namuchitira chipongwe nati, “Tikulonjereni Mfumu ya Ayuda.”
Boka po ngabatengeneza lukamba lyene mimimwa ni kulibeka nnani ya ntwe wake, ni kubonikiya nai muluboko lyake lwa kumalyo. Bapigite magoti nnongi yake kaban'geya, kababaya, “Twenda kusalimu, Mpwalumea Ayahudi?”
30 Anamuthira malovu ndipo anatenga ndodo namumenya nayo pa mutu mobwerezabwereza.
Ngaba muniya mata, ngatola nainkabankombwa mutwe.
31 Atamaliza kumuchitira chipongwe, anamuvula malaya aja namuveka malaya ake aja napita naye kokamupachika.
Muda kabayendelya kunkebei gaba mwula ngobo yake, nganongoya yenda kukongela.
32 Pamene gululi linkatuluka ndi Yesu, anakumana ndi munthu wochokera ku Kurene dzina lake Simoni ndipo anamuwumiriza kunyamula mtanda.
Pabapitike panja, bamweni mundu yumo boka Krene lina lyake Simeoni, batikunlasimisha alongwane nabo lenga atweti nsalaba wake.
33 Anafika ku malo wotchedwa Gologota amene atanthauza kuti malo a bade la mutu.
Pabaikite pandu papakemelwage Goligotha, mana yake, “semu yalipakala lya ntwe.”
34 Pamenepo anamupatsa vinyo wosakaniza ndi ndulu kuti amwe; koma atalawa anakana kumwa.
Kabampei siki yayengabanike ni nongo aywe. lakini paipayite nywele kwaa.
35 Atamupachika Iye, anagawana zovala zake pochita maere.
Muda kabansulubisha, bangine ngobo yake kwa kwipigya kura.
36 Ndipo anakhala pansi namulonda Iye.
Na batitama ni kunnola.
37 Pamwamba pa mutu wake analembapo mawu osonyeza mlandu wake akuti, “uyu ndi yesu, mfumu ya ayuda.”
Nnani ya ntwe wake paandikilwe gastakilwe kangasomeka, “Ayo nga Yesu, mpwalume Ayahudi.”
38 Achifwamba awiri anapachikidwa pamodzi ndi Iye, mmodzi kudzanja lamanja wina kudzanja lamanzere.
Anyang'anyi abele batikwakongela pamope ni ywembe, yumo upande wa kumalyo ni ywembe wa kunkeya.
39 Ndipo amene amadutsa anamunenera mawu a chipongwe, akupukusa mitu yawo.
Balo bababile kabapeta palobende kaban'geya, kabatikisa mitwe gabe,
40 Ndipo anati, “Iwe amene ungapasule Nyumba ya Mulungu ndi kuyimanga masiku atatu, dzipulumutse wekha! Tsika pa mtandapo ngati ndiwe Mwana wa Mulungu!”
no baya, “Wenga wa upalange kulibomwana hekalu ni kulichenga kwa masoba gatatu, “Wilopwe wa mwene! Mana itei wa mwana wa Nnongo, uuluke pae uboke mu'nsalaba!”
41 Chimodzimodzinso akulu a ansembe, aphunzitsi amalamulo ndi akuluakulu anamuchitira chipongwe.
Kati ya hali yeyelo akolo ba makuhani babile bakin'geya, pamope ni baandishi ni apindo, no baya,
42 Iwo anati, “Anapulumutsa ena koma sangathe kudzipulumutsa yekha! Ndi mfumu ya Israeli! Mulekeni atsike pa mtanda ndipo tidzamukhulupirira Iye.
Aokowile banansima, lakini aweza kwaa kwilopwa mwene. Jwembe mpwalume Ayahudi. Auluke pae boka munsalaba, nga twamwamini.
43 Amadalira Mulungu, mulekeni Mulunguyo amupulumutse tsopano ngati akumufuna pakuti anati, ‘Ndine Mwana wa Mulungu.’”
Atikuntumaini Nnongo, leka Nnongo anopwe nambi yambe mana kapala, kwa mwanja atibaya Nenga na mwana wa Nnongo.”
44 Momwemonso mbala zimene zinapachikidwa naye pamodzi zinamuneneranso zachipongwe.
Na balo anyang'anyi babauyongilwe pamope ni ywembe balongei makowe gakun'geya.
45 Kuyambira 12 koloko masana mpaka 3 koloko, kunachita mdima pa dziko lonse.
Buka saa sita kwabi ni lubendo nnema wote mpaka saa tisa.
46 Ndipo nthawi ili ngati 3 koloko, Yesu analira mofuwula nati, “Eloi, Eloi, lama sabakitani!” Kutanthauza kuti, “Mulungu Wanga, Mulungu Wanga, mwandisiyiranji Ine?”
Payaiikite saa tisa, Yesu kalela kwa lilobe likolo, “Eloi, Eloi, lama thabakithan?” mana yake Nnongo wango, Nnongo wango, mbona wenda nileka?”
47 Ena a oyimirira pamalopo atamva izi anati, “Akuyitana Eliya.”
Wakati woo baadhi yabe babile bayemi palo kababekaniya, kababaya, “Ankema Eliya.”
48 Mmodzi wa iwo anathamanga natenga chinkhupule. Anachidzaza ndi vinyo wosasa, nachizika ku mtengo namupatsa Yesu kuti amwe.
Mara jimo yumo ywabe atibutuka yotola sifongo kwitweleya kinyo kikale, ngabaibeka nnani ya nkongo ni kumpeya anywe.
49 Koma ena onse anati, “Mulekeni tiyeni tione ngati Eliyayo abwere kudzamupulutsa.”
Nababaigalile kabakiya, “Muneke kichake, lulole panga Eliya apala isa kunopwa.”
50 Ndipo pamene Yesu analiranso mofuwula, anapereka mzimu wake.
Boka po Yesu atilela kae kwalilobe likolo na awile.
51 Pa nthawi imeneyo chinsalu chotchinga cha mʼNyumba ya Mulungu chinangʼambika pakati kuyambira pamwamba mpaka pansi. Dziko linagwedezeka ndipo miyala inangʼambika.
Linga, pazia lya hekalu ngalipapwanike ipande ibele boka kunani mpaka pae. Ni nnema watilendema na miamba yatipapwanika ipande.
52 Manda anatsekuka ndipo mitembo yambiri ya anthu oyera mtima amene anafa inaukitsidwa.
Makaburi ngayongoka, na yega ya atakatifu banansima babaginjike kabayoka buka mu kiwo.
53 Anatuluka mʼmanda mwawo, ndipo chitachitika chiukitso cha Yesu, anapita mu mzinda woyera naonekera kwa anthu ambiri.
Batipita mumakaburi baada ya kuyoka kwabe, kabayingii mu mji mpeletau, batibonekana na bandu banyansima.
54 Mkulu wa asilikali ndi amene ankalondera Yesu ataona chivomerezi ndi zonse zinachitika, anachita mantha, ndipo anati, “Zoonadi, uyu anali Mwana wa Mulungu!”
Bai yolo akida ni balo bababile kabannola Yesu babweni lilendemo ni makowe goti yapangike palo, batiyogopa muno no baya, “Kweli ayo abile mwana wa Nnongo.'
55 Amayi ambirimbiri amene ankasamalira Yesu ankaonerera ali patali. Iwo anamutsatira Yesu kuchokera ku Galileya.
Alwawa banansima babankengime Yesu boka Galilaya linga kumudumia babile palo kabanlolekeya boka kutalu.
56 Pakati pawo panali Mariya wa ku Magadala, Mariya amayi ake Yakobo ndi Yosefe ndi amayi a ana a Zebedayo.
Nkati yabe abile Mariamu magdarena, Mariamu mao bake Yakobo na Joseph, na mao bake Zebedayo.
57 Pamene kumada, kunabwera munthu wolemera wa ku Arimateyu dzina lake Yosefe amene anali wophunzira wa Yesu.
Paikite kitamunyo, aichi mundu tajiri boka Arimathayo, lina lyake Yusufu, nembe kae ywabile mwanapunzi wa Yesu.
58 Anapita kwa Pilato kukapempha mtembo wa Yesu, ndipo Pilato analamula kuti uperekedwe kwa iye.
Anyendeli Pilato kunnoba bwega wa Yesu, Pilato atilagya apeyelwe.
59 Yosefe anatenga mtembowo, nawukulunga nsalu yabafuta.
Yusufu apeyilwe bwega ni aubilingile ni ngobo ya sufi inoyite,
60 Ndipo anawuyika mʼmanda ake atsopano amene anasema mu thanthwe, natsekapo ndi mwala waukulu pa khomo la mandawo nachokapo.
Ayei kusika mulikaburi lya yambe lyake atikulichonga muliwe. Ngaimbiliya liwe likolo ngaliwekelya pannyango wa likaburi kaboka kachake.
61 Mariya wa Magadala ndi Mariya wina anakhala pansi moyangʼanizana ndi mandawo.
Mariamu magdarena ni Mariamu yolo ywenge babile palo, watitama kabalolekeya kulo kulikaburi.
62 Litapita tsiku lokonzekera Sabata, mmawa mwake, akulu a ansembe ndi Afarisi anapita kwa Pilato.
Lisoba lyenge lyabile lya maandalio, akolo ba makuhani na Mafarisayo batikwembana pamope kwa Pilato.
63 Iwo anati, “Bwana takumbukira kuti munthu wonyenga uja akanali ndi moyo anati, ‘Pakatha masiku atatu ndidzauka.’
Kabammakiya, “Ngwana, tukomboki panga wakati yolo mmocho abile nkoti, atibaya,'Baada ya masoba ga tatu alowa yoka kae,'
64 Choncho lamulirani kuti manda ake atetezedwe mpaka pa tsiku lachitatu. Chifukwa tikapanda kutero, ophunzira ake angabwere kudzaba mtembo wake ndipo angawuze anthu kuti waukitsidwa kwa akufa. Ndipo chinyengo chomalizachi chidzakhala choyipa kwambiri kusiyana ndi choyamba chija.”
Kwa eyo ulangi panga likaburi bakalilende libesalama mpaka masoba gatatu, Yalowa wezekana, anapunzi bake baweza kun'yiba no baya kwa bandu, atiyoka boka mu kiwo! no ubocho wa mwisho walowa mbaya kuliko wa kwanza.
65 Pilato anayankha kuti, “Tengani mlonda kalondereni monga mudziwira.”
Pilato kaayangwa, “Mutole alinzi. Muyende mkapange kati mwa muweza.
66 Tsono anapita nakatseka manda kolimba ndi kuyikapo chizindikiro ndipo anayikapo mlonda.
Ngabatiyenda no kulipanga likaburi panga salama liwe balikombwi muhuri na kubeka alinzi.