< Mateyu 25 >

1 “Nthawi imeneyo ufumu wakumwamba udzafanizidwa ndi anamwali khumi amene anatenga nyale zawo napita kukakumana ndi mkwati.
He wode salo kawotethi mishira mokanas xomppe oykidi kezida tammu gellaota milataysu.
2 Asanu anali opusa ndipo asanu ena anali ochenjera.
He tammatappe ichachu gela7oti eyata, hankko ichachati qasse eraata.
3 Opusawo anatenga nyale zawo koma sanatenge mafuta;
Eyati kuraze xomppe oykida shin wurikko qolana hara nagge lamba oykibeytena.
4 koma ochenjerawo anatenga mafuta awo mʼmabotolo pamodzi ndi nyale zawo.
Erati gidkko ba kurazezara wurikko gujana lagge lammba hara xarmusen oykidda.
5 Mkwati anachedwa ndipo onse anayamba kusinza nagona.
Machiyo ekkana mishiray yonta gam7in dhiskoy dexin asay wurikka dhiskidees.
6 “Pakati pa usiku kunamveka kufuwula kuti, ‘Onani Mkwati! Tulukani kuti mukakumane naye!’
Gidi gidoth gidishin mishrazi yes kezidi moki ekitte giza xeyssa qalay siyetidees.
7 “Pamenepo anamwali onse anadzuka nayatsa nyale zawo.
Hessa wode gela7oti wurikka dendidi ba xomppe xomppe oythethone gigeteth oykida.
8 Opusawo anati kwa ochenjerawo, ‘Tipatseniko mafuta anu; nyale zathu zikuzima.’
Dogati erata nu xomppey to7ana giza gish inte lambappe nus immitte gida.
9 “Ochenjerawo anayankha, nati, ‘Ayi sangakwanire inu ndi ife. Pitani kwa ogulitsa mafuta ndi kukadzigulira nokha.’
Era gela7oti istas zaridi nuss diza lambay nusara intessaranne intesara gidonta gish bidi lamba bayzizaytappe intess shamitte gida.
10 “Koma pamene ankapita kukagula mafutawo, mkwati anafika. Anamwali amene anali okonzeka aja analowa naye pamodzi mʼnyumba ya phwando la ukwati. Ndipo khomo linatsekedwa.
Isti lamba shamna bida wode mishrazi gakiwodhidees. Kasse gigeti utidda gela7oti bulacha so izara gelida, kareykka gordetidees.
11 “Pambuyo pake enawo anabwera nati, ‘Ambuye! Ambuye! Titsekulireni!’
Guth gam7ishe hakko gela7oti yidi “Godo Godo kare nuss doy7a” gida.
12 “Koma iye anayankha kuti, ‘Zoonadi, ine ndikuwuzani kuti sindikukudziwani.’
Izikka zaridi “ta intess tumu gays ta intena erikke” gidees.
13 “Choncho khalani odikira, popeza simudziwa tsiku kapena nthawi.”
Hessa gish yana galasa woykko sateza inte eronta gish gigetidi nagite.
14 “Komanso udzafanizidwa ndi munthu amene ankapita pa ulendo, ndipo anayitana antchito ake nawasiyira chuma chake.
Xoossa kawotethi bess dizaz wursi ba ashikaratas hadara immidi hara dere bana dendida issi ass milatees.
15 Wina anamupatsa ndalama 5,000, kwa wina 2,000 ndi kwa wina 1,000. Aliyense monga mwa nzeru zake. Pamenepo anapita pa ulendo wake.
ashikaratas isas issas istta wolqama mala gigisidi issas ichachu shi birra, issas namm7u shi bira, hankoysas qasse issi shi birra immidi bidees.
16 Munthu amene analandira ndalama 5,000 uja, anapita nthawi yomweyo nachita nazo malonda napindula 5,000 zina.
Ichachu shi birra ekida adezi herakka mishan zal7e oykidi hara ichachu shi birra tirpisidees.
17 Chimodzimodzinso amene analandira 2,000 uja anapindula 2,000 zina.
Qssekka namm7u shi birra ekidaysi hara namm7u shi birra wodhisidees.
18 Koma munthu amene analandira 1,000 uja, anapita nakumba dzenje nabisapo ndalama ya mbuye wake.
Issi shi birra ekidaysi ba goda bira bitan magidi qotidees.
19 “Patapita nthawi yayitali, mbuye wa antchitowo anabwera nawayitana kuti afotokoze chimene anachita ndi ndalama zija.
Ashikarata goday ba bidason daro wode gamm7i simidi misha istara shalagetidees.
20 Munthu amene analandira ndalama 5,000 uja anabweretsa 5,000 zina nati, ‘Ambuye munandisungitsa 5,000, taonani ndapindula 5,000 zinanso.’
Ichachu shi birra ekida ashikaray hara ichachu shi birra wodhsidaysa ekki yidi godo ne tass ichachu shi birra imadasa shin hekko hayssa ta harra ichachu shi bira wodhisadis gidees.
21 “Ambuye ake anayankha nati, ‘Wachita bwino, wantchito wabwino ndi wokhulupirika iwe! Wakhala wokhulupirika pa zinthu zochepa; ndidzakuyika iwe kukhala woyangʼanira zinthu zambiri. Bwera, udzakondwere pamodzi ndi mbuye wako!’
Iza godaykka lo7o othadasa neno lo7o ammanetida ashikarazo ne gutha mishan amanetida ass gidida gish ta nena daro misha bolla shuumana, gede ne goda ufaysaso gela gidees.
22 “Munthu amene anali ndi ndalama 2,000 uja anabweranso nati, ‘Ambuye munandisungitsa 2,000, onani, ndapindula 2,000 zinanso.’
Hessathokka namm7u shi birra ekkidaysi godazakko shiqidi godo ne tass namm7u shi birra immadasa shin hekko hara namm7u shi birra wodhisadis gidees.
23 “Mbuye wake anayankha nati, ‘Wachita bwino, wantchito wabwino ndi wokhulupirika! Wakhala wokhulupirika pa zinthu zochepa; ndidzakuyika kukhala woyangʼanira zinthu zambiri. Bwera, udzakondwere pamodzi ndi mbuye wako!’
Godazikka lo7ethadasa hayso loo7one tass ammanetida ashikarazo neni guthan amanetidade gidida gish ta nena daro misha bolla shuumays, gede ne goda ufaysaso gela gidees.
24 “Kenaka munthu amene analandira ndalama 1,000 uja anabwera nati, ‘Ambuye ndinadziwa kuti ndinu munthu wowuma mtima, amene mumakolola pamene simunadzale ndi kututa kumene simunafese.
Issi shi birra ekkida ashikaray sniqidi godo neni zeronta soppe maxizadene lalonta soppe shishiza minxe iita ass gididaysa ta erays.
25 Choncho ndinachita mantha ndipo ndinapita ndi kukabisa ndalama yanuyo pa dzenje. Onani, si iyi ndalama yanu ija.’
Hessa gish ta babada bitta bokkada ne birra bokkida ollan mogada qotadis, ne miish nesssa beya he7i gidees
26 “Mbuye wake anayankha nati, ‘Iwe wantchito woyipa ndi waulesi! Iwe umadziwa kuti ndimakolola pamene sindinadzale, ndi kututa kumene sindinafese.
Iza goday zaridi hayso iita azala ashikarazo tani zerontasoppe maxizade lalontasoppe shishizade gididaysa ne eray?
27 Bwanji sunayike ndalama yanga kwa osunga ndalama kuti ine pobwera ndidzalandire ndalama yangayo pamodzi ndi chiwongoladzanja?
Histin ta simma yiza wode ta misha yelora ta ekkana mala tirpisi zal7iza asas ne immanas besseseshin gidees.
28 “‘Mulandeni ndalamayo, ndipo patsani iye amene ali ndi ndalama 10,000.
Ane ha7i iza shi birra ekidi tammu shi biray dizadess immitte.
29 Pakuti aliyense amene ali nazo adzapatsidwa zambiri, ndipo adzakhala nazo zochuluka. Aliyense amene alibe adzalandidwa ngakhale chimene ali nacho.
Dizades gujistanane dari dari bana bayndadeppe he diza guthayiyakka izappe ekista gidana.
30 Ndipo muponyeni wantchito wopanda phinduyu kunja, ku mdima kumene kudzakhala kulira ndi kukukuta mano.’”
Haysa go7ay baynda ashikara gede yekizasone achey garcetizaso heni karen diza dhumman kesi yegitte gidees.
31 “Pamene Mwana wa Munthu adzabwera mu ulemerero wake, pamodzi ndi angelo ake onse, adzakhala pa mpando waufumu mu ulemerero wakumwamba.
Assa nay ba kitanchata wursora bonchon yiza wode ba boncho zuppane bolla utana.
32 Mitundu yonse ya anthu idzasonkhanitsidwa pamaso pake, ndipo adzawalekanitsa iwo wina ndi mnzake monga mʼbusa amalekanitsa nkhosa ndi mbuzi.
Derey wuri iza sinthi shiqana izikka mehe hemiza uray desh dorsappe qori shkiza mala asa issa issape qori shakana.
33 Adzayika nkhosa ku dzanja lake lamanja ndi mbuzi ku lamanzere.
Dorsata izas oshacha bagara deshata hadirsa bagara essana.
34 “Pamenepo mfumu idzati kwa a ku dzanja lamanja, ‘Bwerani inu odalitsika ndi Atate anga; landirani ufumu umene unakonzedwa chifukwa cha inu kuyambira pachiyambi cha dziko.
He wode kawoy oshacha bagara dizayta “inte ta aaway intena anjidayti ha yite, alamey medhetosoppe intes gigetida kawotetha latitte gana.
35 Pakuti ndinali ndi njala ndipo munandipatsa chakudya, ndinali ndi ludzu ndipo munandipatsa madzi akumwa, ndinali mlendo ndipo munandilandira,
Gasoykka tani gafin tana muzidista, ta sametin tana ushidista, ta immatha gidada yin tana moki ekidista.
36 ndinali wausiwa ndipo munandiveka, ndinali wodwala ndipo munandisamalira, ndinali ku ndende ndipo inu munandiyendera.’
Ta kalotin tana mayzidista, ta saketin tana hargisidista, ta qashetin tana oychidista.
37 “Ndipo olungamawo adzamuyankha kuti, ‘Ambuye ndi liti tinakuonani muli ndi njala ndipo tinakudyetsani, kapena ludzu ndipo tinakupatsani madzi akumwa?
Xillotikka zaridi “Godo ne gafin nena ayde muzidoni?, woykko ne samotin ayde beydi nena ushidoni?
38 Ndi liti tinakuonani muli mlendo ndipo tinakulandirani, kapena wa usiwa ndipo tinakuvekani?
Nu ayde nena beydi immathateth mokidoni? woykko ayde ne kalotin beydi nena mayzidoni?
39 Ndi liti tinakuonani mutadwala kapena ku ndende ndipo tinakuyenderani?’
Hessathokka ne saketin woykko qachetin ayde beydi nena oychidoni gana.
40 “Mfumu idzayankha kuti, ‘Zoonadi, ndikuwuzani kuti chilichonse chimene munachitira mmodzi wa abale anga onyozekawa munandichitira Ine.’
Kawoykka zaridi ta intes tumu gays hayta lafa gidida ta ishatappe isades inte tass othida mala gana.
41 “Pamenepo adzanena kwa akumanzere kwake kuti, ‘Chokani kwa Ine, inu otembereredwa, pitani ku moto wosatha wokonzedwera mdierekezi ndi angelo ake. (aiōnios g166)
Qassekka hadirsa bagara dizaytas inteno qangetidayto tappe shaketidi Dabulosasine iza kitanchatas gigetida medhina taman bitte gana. (aiōnios g166)
42 Pakuti ndinali ndi njala ndipo simunandipatse chakudya, ndinali ndi ludzu ndipo simunandipatse madzi akumwa,
Gasoykka ta gafin tana muzibeykkista, ta samotin tana ushibeykista,
43 ndinali mlendo koma inu simunandilandire, ndinali wa usiwa koma simunandiveke, ndinali wodwala komanso ku ndende simunandisamalire.’
tana immathateth mokibeykista. ta kalotin tana mayzibeyketta, ta saketinine qashetin tana oychibeyketta.
44 “Iwo adzayankha kuti, ‘Ambuye ndi liti tinakuonani muli ndi njala kapena ludzu kapena mlendo kapena wausiwa kapena wodwala kapena mʼndende, ndipo kuti sitinakuthandizeni?’
Istika zaridi godo ne gafin woykko ne samotin woykko ne immath gidin woykko ne kalotinine ne sakketin woykko ne qachetin nu nenna beydi ayde ness gakibeykoni? gana.
45 “Iye adzayankha kuti, ‘Zoonadi, ndikuwuzani kuti chilichonse chimene simunachitire mmodzi wa abale anga onyozekawa simunandichitire Ine.’
He wode izikka istas zaridi ta intees tumu gays haninta lafa ta ishatappe issadees inte othonta agidaysi tass inte othonta agida mala gana.
46 “Amenewa adzapita ku chilango chosatha pamene olungama ku moyo wosatha.” (aiōnios g166)
Heyti gede medhina pirdan bana xilota gidikko medhina deyokko bana. (aiōnios g166)

< Mateyu 25 >