< Mateyu 24 >

1 Yesu anatuluka mʼNyumba ya Mulungu ndipo akuchoka ophunzira ake anadza kwa Iye ndi kumuonetsa mamangidwe a Nyumbayo.
Yesu aulukile mwiekalu na genda jae. Abhweigisibhwa bhae bhamulubhile nokumwelesha inyumba ya Iyekalu.
2 Iye anawafunsa kuti, “Kodi mukuona zinthu zonsezi? Zoonadi, Ine ndikuwuzani kuti palibe mwala pano umene udzasiyidwe pa unzake; uliwonse udzagwetsedwa pansi.”
Nawe abhasubhishe no kubhabhwila,” Mtakugalola amagambo aga gone nichimali enibhabhwila ati litalio ebhui linu elisigalao ingulu yelidi linu litalifumibhwa.”
3 Pamene Yesu anakhala pansi pa phiri la Olivi, ophunzira ake anabwera kwa Iye mwamseri nati, “Tiwuzeni, kodi izi zidzachitika liti, ndipo chizindikiro cha kubwera kwanu ndi zizindikiro za kutha kwa dziko zidzakhala chiyani?” (aiōn g165)
Na ejile eyanja kuchima ja mujeituni, abhweigisibhwa bhae bhamulubhile kwo kwitebha nibhaika ati, “chibhwile, amagambo ganu galibha lii? Nichinuki chilibha chibhalikisho Cho kuja kwao no bhutelo bhwechalo?” (aiōn g165)
4 Yesu anayankha kuti, “Onetsetsani kuti wina asakunyengeni.
Yesu abhasubhishe no kubhabhwila ati, “Mukabhuke ati atalija munu akabhayabhya.
5 Pakuti ambiri adzabwera mʼdzina langa nadzati, ‘Ndine Khristu,’ ndipo adzanyenga ambiri.
Okubha bhafu bhalija kwisina lyani. Nibhaika ati,' Anye nanye Kristo', abhabhayabhya bhafu.
6 Mudzamva za nkhondo ndi mbiri za nkhondo, koma onetsetsani kuti musadzidzimuke nazo. Zotere ziyenera kuchitika, koma chimaliziro sichinafike.
Mulyungwa lilemo no bhumenyi bho bhulemo. Mulolenga mutalija kubha na bhubha okubha amagambo ganu gatalilema kubhao; Nawe obhutelo obhubha bhuchali.
7 Mtundu ndi mtundu udzawukirana, ndipo ufumu ndi ufumu udzawukirana. Kudzakhala njala ndi zivomerezi mʼmalo osiyanasiyana.
Okubha liyaanga Lilimuka kwiyanga lwejabho, no bhukama bhulija kubhukama bhwejabho. Ilibhao ijala na ganyamutikima gaisi mabhala na mabhala.
8 Zonsezi ndi chiyambi chabe cha zowawa.
Nawe amagambo ganu gone nibhwambilweela bho bhusungu bho kwibhula.
9 “Pamenepo adzakuperekani kuti mukazunzidwe ndi kuphedwa, ndipo mitundu yonse idzakudani chifukwa cha Ine.
Nio bhalibhasosha muje okunyasibhwa no kubheta. Muligengwa na maaga gone kulwaijuno ya lisina lyani.
10 Pa nthawi imeneyo ambiri adzasiya chikhulupiriro ndipo adzadana ndi kuperekana wina ndi mnzake,
Nio abhafu bhalikujula no kulomelana iniku na bhaliyambana abhene kwa bhene.
11 ndipo aneneri onama ambiri adzaoneka ndi kunyenga anthu ambiri.
Abhalangi bhafu abholulimi bhalija no kubhajiga bhwafu.
12 Chifukwa cha kuchuluka kwa zoyipa, chikondi cha ambiri chidzazirala,
kusonga obhunyamuke bhuliyongesha, okwenda kwabhafu okunyilila.
13 koma wopirira kufikira chimaliziro adzapulumuka.
Nawe unu alikomesha okukinga kubhutelo, alikisibhwa.
14 Ndipo uthenga wa ufumu udzalalikidwa ku dziko lonse lapansi ngati umboni kwa mitundu yonse, ndipo pomwepo chimaliziro chidzafika.”
Chinu echigambo Cho bhukama chisimulwa muchalo chone uti bhubhambasi kumaaga gonna. Mbe nio obhutelo nibhukinga.
15 “Tsono mukadzaona chinthu chonyansa chosakaza chitayima pamalo oyera chimene anayankhula mneneri Danieli, owerengayo azindikire.
Mbe nawe, mulibha mwalola echifululusho cho kusimagisha, linu lyaikwilwe no Mulagi Danyeli limeleguyu anu elele (unu kasoma asombokelwe),
16 Pamenepo amene ali ku Yudeya athawire ku mapiri.
Nio bhanu bhaliga mu Yuda bhabhilimile muchima.
17 Yemwe ali pa denga la nyumba yake asatsike kukatulutsa chinthu chilichonse mʼnyumba.
Unu ali ingulu yo lusala lwa inyumba asige okutuka, okwika amwi okugega chone chone okusoka munyumba yae,
18 Yemwe ali ku munda asapite kukatenga mkanjo wake.
Na unu ali mwisambu asige kusubha kugenga ingubho yae.
19 Kudzakhala koopsa kwambiri masiku amenewo kwa amayi oyembekezera ndi kwa oyamwitsa!
Mbe nawe jilibhabhona bhaliya abho bhali na bhana na bhalia abho abhanen'ya musiku ejo!
20 Pempherani kuti kuthawa kwanu kusadzachitike nthawi yozizira kapena pa Sabata.
Musabhwega ati okubhilima kwemwe kutalibha musiku ja ibeo amwi kulusiku lwa isabhato.
21 Popeza kudzakhala masautso aakulu, omwe safanana ndi ena ali onse chiyambireni cha dziko lapansi mpaka lero lino ndipo sadzafanananso ndi ena.
Kulwo kubha ilibhao inyanko nene, inu ichaliga kubhao kusokelela kubhwambilo bhwa insi okukinga lelo, na nolwo italibhao lindi.
22 Ngati masiku amenewo sakanafupikitsidwa, palibe mmodzi akanapulumuka, koma chifukwa cha osankhidwawo masiku amenewo adzafupikitsidwa.
Ka jisiku ejo jichilema okeibhwako, atakabhweyeo oyo akakisibhwe nawe kulwa bhasolwa, jisisiku ejo jilikeibhwa.
23 Pa nthawi imeneyo ngati wina adzati kwa inu, ‘Onani, Khristu ali pano!’ Kapena, ‘Uyo ali ukoyo!’ Musakhulupirire.
Nio ilibha munu wone wone akabhabhwila ati 'Lola, 'Kristo alyanu! Amwi, 'Kristo' ali elia Musige okwilisha emisango ejo.
24 Chifukwa akhristu onama ndi aneneri onama adzaoneka ndipo adzachita zizindikiro zazikulu ndi zodabwitsa kuti akanyenge ngakhale osankhidwawo ngati kukanakhala kotheka kutero.
Ku lwo kubha abha kristo bholulimi na bhalagi bholulimi bhalija ni bholesha jibalikisho nene ne bhilugusho, koleleki bhabhayabhye, ka labha bhakatula nolwo abhasolwa.
25 Onani, ndakuwuzani izi nthawi isanafike.
Mbe nimulole natangata okubhakabhusha inyuma ya magambo ago gachali kubhonekana
26 “Ndiye ngati wina akuwuzani inu kuti, ‘Uyo ali ku chipululu,’ inu musapiteko; kapena akati, ‘Uyu ali kuno mʼchipinda chamʼkati,’ musakhulupirire.
Ku lwejo, nolwo bhakabhabhwila ati, “Kristo ali mwipoli, mutaligeda eyo mwipoli amwi ni mulole, ali munyumba, mwasiga okwikilisha emisango ejo.
27 Monga momwe mphenzi ingʼanima kuchokera kummawa kupita kumadzulo, momwemonso kudzakhala kubwera kwa Mwana wa Munthu.
Okubha lwa kutyo olulabhyo olumulika okusoka ebhutuluka nilwolesha okukiga ebhugwa, nikwo kutyo kulibha okuja kwo mwana wo munu.
28 Kulikonse kuli chinthu cha kufa, makwangwala adzasonkhanako.
One one anu guli omutumbi, eyo niyo jipungu ejikofyanyisha
29 “Akadzangotha mavuto a masiku amenewo, “‘dzuwa lidzadetsedwa, ndipo mwezi sudzawala; nyenyezi zidzagwa kuchokera kumwamba, ndipo mphamvu za mmwamba zidzagwedezeka.’
Nawe alibha yawa inyako inene yajisiku jiliya, lisubha lilitulilwao omwilima, okwesi kutakusosha bhwelu bhwakwo, jijota jililagala okusoka kulwile, na managa mulwile galisingisibhwa.
30 “Pa nthawi imeneyo chizindikiro cha Mwana wa Munthu chidzaoneka mlengalenga, ndipo mitundu yonse ya pa dziko lapansi idzalira. Idzaona Mwana wa Munthu akubwera ndi mitambo, mphamvu ndi ulemerero waukulu.
Mbe nio echibhalikisho cho mwana wo munu chilibhonekana kulwile, najingada jone jechalo jililila nijinega. Bhalimulola omwana wo munu naja mumele aga kulwile kwa managa na likusho lyafu.
31 Ndipo adzatuma angelo ake, ndi kulira kwa lipenga kwakukulu, nadzasonkhanitsa osankhidwa ake kuchokera ku mphepo zinayi, ndi kuchokera kumathero a thambo kufika mbali ina.
Alibhatuma bhamalaika bhae no bhulaka bhunene obhwaing'ombi, nibho bhulibhakumanya amwi abhasolwa bhae bhokusoka mbala ena ejechalo, okusoka bhutelo bhumwi bho lwile okukinga kubhundi.
32 “Tsopano kuchokera ku mtengo wamkuyu phunzirani ichi: Pamene uyamba kuphukira, masamba ake akatuluka, mumadziwa kuti dzinja layandikira.
Mwiigile lisomo okusokana na liti litini. Litabhi likasebhuka no kusosha amabhabhi, mumenye ati olwanda luli yei.
33 Momwemonso, pamene mudzaona zinthu zonsezi mudzadziwe kuti ali pafupi pa khomo penipeni.
Ni kwo kutyo, mulilola amagambo ganu gone, jibheile okumenya ati ali yei kumilyango.
34 Zoonadi, ndikuwuzani kuti mʼbado uwu sudzatha mpaka zinthu zonse zitachitika.
Ni chimali enibhabhwila, olwibhulo lunu lutaliwao, okukingila amagambo gone ganu agabha gabhonekene.
35 Kumwamba ndi dziko lapansi zidzatha, koma mawu anga sadzatha.”
Olwile na nsi bhiliwao, tali emisango jani jitaliwao chimwi.
36 “Palibe amene adziwa za tsikulo kapena nthawi, angakhale angelo akumwamba, angakhale Mwana, koma Atate okha.
Nawe ebhyo lusiku lulia na isaa atalio munu unu amenyele, nakabhee nolwo bhamalaika bhamulwile nolwo omwana, Tali lata omwene enyele.
37 Monga momwe zinalili nthawi ya Nowa, momwemonso zidzatero pobwera kwa Mwana wa Munthu.
Na ka lwakutyo jaliga jili musiku ja Nuu, nikwo ilibha okuja kwo mwana wo munu.
38 Pakuti masiku amenewo chisanafike chigumula, anthu amadya ndi kumwa, kukwatira ndi kukwatiwa, mpaka tsiku limene Nowa analowa mʼchombo;
kulwo kubha musiku ejo inyuma ya dulima abhanu bhaliga nibhalya no kunywa, nibhatwala no kutwalwa no kukingila olusiku lulia olwo engila mungalabha,
39 ndipo sanadziwe za chimene chikanachitika mpaka pamene chigumula chinafika ndi kuwamiza onse. Umu ndi mmene zidzakhalira pobwera kwa Mwana wa Munthu.
Na bhatamenyele chinu chone chone okukingila iduluma olwo yejile nibhagega bhone -nikwo kulibha okuja kwo mwana wo munu.
40 Amuna awiri adzakhala mʼmunda; wina adzatengedwa ndi wina adzatsala.
Niwo bhanu bhabhili bhalibha bhali mwisabhu- oumwi aligengwa no umwi alisigala inyuma.
41 Amayi awiri adzakhala akusinja pa mtondo; wina adzatengedwa ndi wina adzatsala.
Abhagasi hhabhili bhalibha nibhasya bhali amwi -oumwi aligegwa no oumwi kasigala.
42 “Chifukwa chake yangʼanirani, popeza simudziwa tsiku lanji limene Ambuye anu adzabwera.
Mbe, nimwegee, kulwo kubha mutakumenya ni lusiku ki lunu alja esobhugenyi wemwe.
43 Koma zindikirani ichi: Ngati mwini nyumba akanadziwa nthawi yanji ya usiku imene mbala imabwera, sakanagona ndipo sakanalola kuti nyumba yake ithyoledwe.
Nawe mumenye chinu ati, chibha kanya nyumba amenyele omwanya na saa ki inu omwifi kejilamo akalindilie na atakekilisishe nyumba yae okwingililwa.
44 Inunso tsono muyenera kukhala okonzeka, chifukwa Mwana wa Munthu adzabwera pa nthawi imene inu simukumuyembekezera.
Ku lwejo, one mwiile okubha mumalilie, okubha omwana wo munu alija mu mwanya gunu mutakwiganilisyamo.
45 “Kodi wantchito wokhulupirika ndi wanzeru amene ambuye ake anamuyika kukhala woyangʼanira antchito a mʼnyumba kuti awapatse chakudya chawo pa nthawi yake ndani?
Mbe niga unu Ali Mulengelesi, omugaya wo bhwenge, unu Esebhugenyi waye amuyae obhukulu ingulu yabho bhali munyumba yae, koleleki abhayane ebhilyo ku mwanya gunu gwiile?
46 Chidzakhala chabwino kwa wantchitoyo ngati mbuye wake pofika adzamupeza akuchita zimenezi.
Ana libhando omugaya oyo, unu Esebhugenyi wae alimusanga nakolaga kutyo omwanya gunu alija.
47 Zoonadi, ndikuwuzani kuti adzamuyika kukhala woyangʼanira katundu wake yense.
Nichimali enibhabhwila ati Esebhugenyi alimutula ingulu ya bhuli chinu echo chili chae.
48 Koma tiyerekeze kuti wantchitoyo ndi woyipa, nati kwa iye yekha, ‘Mbuye wanga akuchedwa kubwera,’
Ka nawe omugaya omubhibhi kaika mumutima gwae, Latabhugenyi wani akola.'
49 nayamba kumenya antchito anzake, nadya ndi kumwa ndi zidakwa.
No okwamba okubhabhuma abhagaya bhae, na akalya no kutamila amwi na bakolwa,
50 Mbuye wa wantchitoyo adzabwera pa tsiku limene iye samamuyembekezera ndi pa nthawi imene iye sakuyidziwa.
Esebhugenyi wae omugaya oyo alija kulusiku lunu atakwiganilisya, na mu saa inu atakuimenya.
51 Adzamulanga koopsa ndipo adzamuyika kokhala anthu achiphamaso, kumene kudzakhala kulira ndi kukukuta mano.”
Esebhugenyi wae alimubhutula mabhala gabhili no kumutula lubhala lumwi amwi na bholulimi, niwo kulibhao okulila na okuguguna ameno.

< Mateyu 24 >

The World is Destroyed by Water
The World is Destroyed by Water