< Mateyu 21 >

1 Akuyandikira ku Yerusalemu anafika ku Betifage pa phiri la Olivi, Yesu anatumiza ophunzira awiri,
U Yesu na wanafunzi wakwe bhahafia karibu Huyerusalemu na wakhawala mpaka Bethfage, hwi gamba ilya mizeituni, nantele u Yesu akhabhawonzya awanafunzi wawele,
2 nawawuza kuti, “Pitani ku mudzi uli patsogolo panu, ndipo mukakangolowa mʼmenemo mukapeza bulu womangidwa ali ndi mwana pa mbali pake. Mukawamasule ndipo mubwere nawo kwa Ine.
akhawawozya, “Walaji hushijiji shishili hwilongolela isala zyezi munza huyanje idogobhi ipinyilwe pala, inyanadango yakwe. Mubhaule na huwalete huline.
3 Wina akakayankhula, mukamuwuze kuti Ambuye akuwafuna, ndipo adzawatumiza nthawi yomweyo.”
Nkha muntu wowonti ahuwawozya lioliontu ahusu elyo, munza, `U Bwana ahubhanza, ` umuntu unyo hani hani anza huwenteshe ahwenze nayo”
4 Izi zinachitika kukwaniritsa zimene zinayankhulidwa ndi mneneri:
Ijambo elyo lyahafumie lilila lyakhayangwilwe na watumi lazima lifumile. Shakhabhawozezye,
5 “Uza mwana wamkazi wa Ziyoni, taona, mfumu yako ikubwera kwa iwe, yofatsa ndi yokwera pa bulu, pa kamwana ka bulu, mwana wa nyama yonyamula katundu.”
Bhawozye abhalendu bhahusayuni, enyhi uumwene wakho hu za humwenyu umwololo akhangaliye idogobhi umwana dogobhi unume, umwana dogobhi umembha.
6 Ophunzirawo anapita nachita monga Yesu anawalamulira.
Nantele awanafunzi bhahasogola nawombhe nanzi u Yesu shabhalajizizye.
7 Anabweretsa bulu ndi mwana wake, nayala zovala zawo pa abuluwo, ndipo Yesu anakwerapo.
Bhakhanetela idogobhi nu mwana dogobhi nawhesha amenda gao humwanya yao, nape u Yesu ahakhala pala.
8 Gulu lalikulu la anthu linayala zovala zawo mu msewu pamene ena anadula nthambi zamitengo ndi kuziyala mu msewumo.
Whinchi bhakhawongeni wakhala amenda gao mwidala, na awamo bhahadumuye amadhanzala afume mumakwi bhahalile mubalabala.
9 Magulu amene anali patsogolo pake ndi amene amamutsatira anafuwula kuti, “Hosana Mwana wa Davide!” “Wodala Iye amene abwera mʼdzina la Ambuye!” “Hosana mmwambamwamba!”
Awhinchi bhabhahatagaliye u Yesu bhala bhabhahafuatile u Yesu bhahabhanjile bhahayanga, “Hosana umwana wa Daudi! Usayhiwilwe uyezela hwitawa lya Bwana. Hosana humwa hani!”
10 Yesu atalowa mu Yerusalemu, mzinda wonse unatekeseka ndipo anthu anafunsa kuti, “Ndani ameneyu?”
U Yesu lwahafia Huyerusalemu, umji ghonti gwakhongopa nayanje aje, “Uno yu nanu?
11 Magulu a anthu anayankha kuti, “Uyu ndi Yesu, mneneri wochokera ku Nazareti.”
“Awhichi wakhayanga, “Onho yu Yesu utumwa, afume Hunazareti ya Hugalilaya.”
12 Yesu analowa mʼdera lina la Nyumba ya Mulungu ndipo anatulutsa kunja anthu onse amene ankachita malonda. Anagubuduza matebulo a osinthira ndalama ndi mipando ya ogulitsa nkhunda.
Nantele u Yesu ahinjila hushiwanza sha Ngolobhe ahawamanyizya hoze wunti bhahakalaga na kazye mshiwanza. Antele ahagwisizye imeza zya bhahakalananga ihela ni vinti vyakhabhakazianga iunda.
13 Iye anawawuza kuti, “Zinalembedwa kuti Nyumba yanga idzatchedwa Nyumba ya mapemphero koma inu mwayisandutsa phanga la anthu achifwamba.”
Akhawawozya, “Isimbwilwe, “Inyumba yane inzakwiziwe nyumba ya puutile, `eshi amwe muyiweshele lipaho lya hupele.”
14 Anthu osaona ndi olumala anabwera kwa Iye mʼNyumba ya Mulungu ndipo anawachiritsa.
Naulele bwawabadiye bhakhalemeye bhahamalila hushibhanza nape akhabhaponizye.
15 Koma akulu a ansembe ndi aphunzitsi amalamulo ataona zodabwitsa zimene anachita, komanso ana akufuwula mʼNyumbayo kuti, “Hosana kwa Mwana wa Davide,” anapsa mtima.
Lakini awagosi wishiwanzya na abhasimbi lwabhakhalola amayele gawombile, na lwabhahovya awana bhabwanga ishongo mshibhaza na ayanje, “Hosana amwana wa Daudi,” bhakhakhatwilwe ni lioyo.
16 Anamufunsa kuti, “Kodi mukumva zimene anawa akunena?” Yesu anayankha nati, “Inde. Kodi simunawerenge kuti, “Kuchokera mʼkamwa mwa ana ndi makanda mwatuluka mayamiko?”
Bhakhamuozezye, uyumvyezye shabhayanga ewa abhantu?” U Yesu akhabhawozya, “Eee! inovyezye, lakini sagamuwahile abhazye afume humalomo gabhana na awasanga bhabhahoha muli indombo kamili?”
17 Ndipo anawasiya natuluka mu mzindawo ndi kupita ku Betaniya, kumene anakagona.
Nantele u Yesu akhawaleha akhawala honze yikhaya huu Bethania na ahagona khuho.
18 Mmamawa, pamene amabwera ku mzinda, anamva njala.
Ishandabhe lwakhawelanga humjini akhali ni nzala.
19 Ataona mtengo wamkuyu mʼmbali mwa msewu, anapitapo koma sanapeze kanthu koma masamba okhaokha. Pamenepo anati kwa mtengowo, “Usadzabalenso chipatso!” Nthawi yomweyo mtengowo unafota. (aiōn g165)
Akhalola ikwi pambembe yi barabara. Akhawala, lakini sagaahapente ahantu humwanya yankwe ila amatundu. Akhaliwozezye, “Usahabhe namadondo wila wila nantele.” Amasala gengo ikwi lila lyahoma. (aiōn g165)
20 Ophunzira ataona zimenezi, anadabwa nafunsa kuti, “Kodi mtengo wamkuyuwu wauma msanga bwanji?”
Abhansukulu lwabhakhalola, bhakhaswinjile na yanje, “Yabhawele ikwi lyomele sheshi sheshikhani?”
21 Yesu anayankha kuti, “Zoonadi, ndikuwuzani kuti ngati muli ndi chikhulupiriro ndipo simukayika, simudzangochita zokha zachitika kwa mkuyuzi, koma mudzatha kuwuza phiri ili kuti, ‘Pita, kadziponye wekha mʼnyanja,’ ndipo zidzachitikadi.
U Yesu akhabhajimbu akhabhawozya lyoli ihumbawozya aje khamli nu lwetekho bila uwonga, sangamzawombe shishiwhumbeshe hwikwi tu, lakini mnzahuwhuzye hata elugamba lyengwe na hulitanje mwidimi igosi na inzawombeshe.
22 Ngati mukhulupirira, mudzalandira chilichonse chimene muchipempha mʼpemphero.”
Lyolyonti lyamza labhe na punte nkhamli nulweuteho munzaposhele.”
23 Yesu analowa mʼNyumba ya Mulungu, ndipo pamene ankaphunzitsa, akulu a ansembe ndi akuluakulu anabwera kwa Iye namufunsa kuti, “Muchita izi ndi ulamuliro wanji ndipo anakupatsani ndani ulamuliro umenewu?”
U Yesu lwakhafika mshibhanza awagosi bha makuhani na bhagogolo bha bhantu wakhamalila lwahamanyizianga, na wakhamozya, “Hungovu wele uwomba amambo enga? Na yu nanu apiye ingovu enzi?”
24 Yesu anayankha kuti, “Inenso ndikufunsani funso limodzi, mukandiyankha, Inenso ndikukuwuzani ndi ulamuliro wa yani umene ndikuchitira izi.
U Yesu ahawajibu na hubhawozye, “Nane ihumba whuzya iswali lyekha. Nkhamuhubozya anje anane iwombo enga hungovu ya nanu.
25 Ubatizo wa Yohane unachokera kuti? Kumwamba kapena kwa anthu?” Anakambirana pakati pawo ndipo anati, “Tikati, ‘Kuchokera kumwamba,’ Iye adzafunsa kuti, ‘Bwanji simunakhulupirire?’
Uwhoziwa wa Yohana- wakhafumile hwii, humwanya au hwa wantu?” Bhanayangana wene, aje, nkhatiyanje whakhafumile humwanya, `anzahutiwhozye shonu sangamwaha mweteshe? `
26 Koma tikati, ‘Kuchokera kwa anthu,’ ife tikuopa anthuwa, pakuti onse amakhulupirira kuti Yohane anali mneneri.”
Nantele nkhatiyanje whakhafumile hwabhantu, `tihuwongopa wishiwaza, sababu whunti bhahunola u Yohana aje yutumi.”
27 Choncho anamuwuza Yesu kuti, “Sitikudziwa.” Pamenepo Iye anati, “Inenso sindikuwuzani kuti ndi ulamuliro wa yani umene ndichitira izi.”
Nantele bhahajibu u Yesu, “Sagatimanye” Akhabhawozya nape nane sangaihumbawhuzya hungovu wele iwhomba amambo ega.
28 “Kodi muganiza bwanji? Panali munthu wina anali ndi ana aamuna awiri. Anapita kwa woyamba nati, ‘Mwanawe pita kagwire ntchito lero mʼmunda wamphesa.’
Eshi msebha yenu? Umuntu yalinawana wawele. Akhabhala hwa weka akhamozya, `Mwanawane, bhala uwombe imbombo hugonda gwi mizabibu,
29 “Iye anayankha kuti, ‘Sindipita,’ koma pambuyo pake anasintha maganizo napita.
ilelo. `Umwana ahajibu na yan sangaimbala, Lakini pamande akhabadilisya isewho zyakwe akhabhala.
30 “Kenaka abambowo anapita kwa mwana winayo nanena chimodzimodzi. Iye anayankha kuti, ‘Ndipita abambo,’ koma sanapite.
Na umuntu ula akhabhala hwamana wabhile humuozye shishila. Umwana ola ahajibu na yanje aje imbala, gosi,' lakini sagawabhala.
31 “Ndani wa awiriwa anachita chimene abambo ake amafuna?” Anamuyankha nati, “Woyambayo.” Yesu anawawuza kuti, “Ndikuwuzani zoonadi, kuti amisonkho ndi adama akulowa mu ufumu wa Mulungu inu musanalowemo.”
Yunanu kati ya wana bhabhile yawhombiole shahwanza uudada wakwe? Bhakhamuzya, “Umwana uwahuande.” U Yesu akhabhawonganya ikondi na bhamalaya bhahaiinjila hwa mwene hwa Ngolobhe shamsele amwe ahwinjile.
32 Pakuti Yohane anabwera kwa inu kuti akuonetseni njira yachilungamo, koma inu simunakhulupirire iye, koma amisonkho ndi adama anamukhulupirira. Koma ngakhale munaona izi, simunatembenuke mtima ndi kumukhulupirira iye.
Huje u Yohana akhenzele hulimwe hwidala liligoloshe, lakini amwe sagamwahaposheye, eobha whunga nya ikodi na bhamalaya bhakhaposheye. Amwe, iwamwakhalola elyo liwhombeha sangamwakha lambihe aje pamande mposhele.
33 “Tamverani fanizo lina: Panali mwini munda amene anadzala mphesa. Anamanga mpanda kuzungulira mundawo, nakumba moponderamo mphesa ndipo anamanga nsanja. Kenaka anabwereketsa munda wamphesawo kwa alimi ena napita pa ulendo.
Tejelezi ufyana ungwamwao. Hwakhali umuntu, umuntu yalini sehemu ingosi iyinsi. Ahatotile amizabibu akhaga wesheye imbanga ahagombile ishombo sha nkhamile idivai, ahazenga iboma lyawalizi, ahapanjizya bhabhalimilila umuzabibu. Ahasongola akhawala insi inyamwao.
34 Pamene nthawi yokolola inakwana, anatumiza antchito ake kwa matenanti aja kuti akatenge zipatso zake.
Uwakati wavune imizabibu lwabhafiha ahabhalajizya abhawomba mbombo hwabhalima amizabibu ahweje amizabibu gankwe.
35 “Alimi aja anagwira antchito ake; namenya mmodzi, napha wina, ndi kumuponya miyala wachitatuyo.
Lakini bhabhalima amizabibu bhahawenga abhawomba mbombo wakwe, bhahakhoma weka bhabuda uwamwao bhakhoma weka na mawe.
36 Kenaka anatumiza antchito ena oposa oyambawo ndipo matenantiwo anawachitira chimodzimodzi.
Nantele ugosi ahatuma abhawomba mbombo abhamwao, winchi hani ashile wala abhahuande, bhabhalima amizabibu bha khawobile shishila.
37 Pomalizira anatumiza mwana wake. Anati adzamuchitira ulemu mwana wanga.
Baada yepo ugosi ula akhatuma umwana wakwe, ahaga, 'Wazahutinishe umwana wane.'
38 “Koma alimiwo ataona mwanayo anati kwa wina ndi mnzake, ‘Uyu ndiye olowa mʼmalo mwa abambo ake. Tiyeni timuphe ndipo titenge cholowa chake.’
Lakini bhabhalima amizabibu lwabhanola usahala ula, bhakhayangana, “Onu yu mrithi, Inzaji, tibude na tenye urithi.'
39 Pamenepo anamutenga namuponyera kunja kwa munda wamphesa namupha.
`Basi bhahatanga hunze mugonda gwi mizabibu na hubude.
40 “Tsono akabwera mwini munda wamphesa adzachita nawo chiyani matenantiwo?”
Jee ugosi wigonda wa mizabibu lwanza ahwenze anza huwawombe wele bhabhalima imizabibu?”
41 Iwo anayankha kuti, “Adzawapha moyipa alimi oyipawo ndipo adzabwereketsa mundawo kwa alimi ena amene adzamupatsa gawo lake la mbewu pa nthawi yokolola.”
Bhakhamuozya, “Anzahubhananganye ewho awantu abhabhibhi, hwidala ikhali hani, na anza panjizye ugonda gwi mizabibu hwa bhakulima abhamwawo wamizabibu, awantu bhabhaza sombe kwajili ya mizabibu lwagazatone.”
42 Yesu anawawuza kuti, “Kodi simunawerenge mʼmalemba kuti: “‘Mwala umene omanga nyumba anawukana, womwewo wasanduka mwala wofunika kwambiri wa pa ngodya. Ambuye wachita izi, ndipo ndi zodabwitsa mʼmaso mwathu.’
U Yesu akhabhawozya, “Aje sangamubhazizye amaandiko, iwe lwabha akhanile awazenje lyabha liwe ligosi lya msingi. Eli kyakhafumile hu Bwana, lishwizisya pamaso gentu?”
43 “Nʼchifukwa chake ndi kukuwuzani kuti ufumu wa Mulungu udzalandidwa kwa inu ndipo udzapatsidwa kwa anthu amene adzabereka chipatso chake.
Eshi ihumbawhuzya, u Umwene wa Ngolobhe unzahungwe agume humwenyu, wanzapelwe bhamunsi bhabhasnga amadondu gankwe.
44 Amene agwa pa mwalawu adzadukaduka, ndipo amene udzamugwere udzamuthudzula.”
Whowhitu yazangwe humwanya yi iwe elyo anzabuduhane buduhane. Lakini whowhunti yalinzahugwele linzahusye.”
45 Akulu a ansembe ndi Afarisi atamva mafanizo a Yesu, anadziwa kuti ankanena iwo.
Abhagosi wishiwanza na Amafarisayo lwawhonvya ishifano shakwe, bhakhamanya aje ahubhayanga wewo.
46 Pamenepo anafuna njira yoti amugwirire, koma anaopa gulu la anthu chifukwa anthu onse ankakhulupirira kuti Iye anali mneneri.
Lakini lwabhanzaga agolosye inyobhe hwa mwene, bhahogope awashibhaza, awantu bhakhamwenyizye aje mtumi.

< Mateyu 21 >