< Mateyu 19 >
1 Yesu atatsiriza kunena zinthu zimenezi, anachoka ku Galileya ndi kupita ku chigawo cha Yudeya mbali ina ya mtsinje wa Yorodani.
Yesusay hasa7i wursidappe guye Galila agidi Yordanose pinthan diza Yihuda awuraja bidees.
2 Magulu akulu a anthu anamutsatira Iye, ndipo iwo anachiritsidwa pomwepo.
Daro derey iza hen kalin izikka harganchata pathidees.
3 Afarisi ena anabwera kwa Iye kudzamuyesa. Anamufunsa Iye nati, “Kodi ndikololedwa kuti mwamuna amuleke mkazi wake pa chifukwa china chilichonse?”
Parsaweti iza pacanas izakko shiqidi ay gasonkka assi ba machcho anjana besize? gidi oychida.
4 Iye anayankha kuti, “Kodi simunawerenge kuti pachiyambi Mulungu analenga iwo, ‘mwamuna ndi mkazi?’
Izikka istas Xoossi koyroppe macane adene medhidaysa nababibeyketi? gidess.
5 Ndipo anati, ‘Pa chifukwa ichi mwamuna adzasiya abambo ake ndi amayi ake nakaphatikana ndi mkazi wake, ndipo awiriwo adzakhala thupi limodzi.’
Qassekka assi awane ayo agidi ba machchira issippe gidees, nam7anykka issi asho gidetes getetidaysi hayssa gedon gidene? gidess.
6 Motero salinso awiri ayi koma mmodzi. Nʼchifukwa chake chimene Mulungu wachimanga pamodzi munthu wina asachilekanitse.”
Nam7ay issi asho atin sinthafe namyu gidetena. Hessa gish Xoossi gathi waxidaysa assi shakofo.
7 Ndipo iwo anamufunsa nati, “Nanga nʼchifukwa chiyani Mose analamula kuti mwamuna azipatsa mkazi wake kalata ya chisudzulo ndi kumuchotsa?”
Istika izas histin Musey assi ba machcho anjidi anjo waraqata izis immidi yedo gidi aazas azazide? gida.
8 Yesu anayankha kuti, “Mose anakulolezani kuti muzisudzula akazi anu chifukwa cha kuwuma mitima kwanu. Koma sizinali chotere kuyambira pachiyambi.
Yesusaykka istas Musey inte wozina mumeteth beydi machcheta inte anjana mla fiqde intes imides atin koyroppe hessamala gidena gidees.
9 Ine ndikuwuzani kuti aliyense amene asudzula mkazi wake, osati chifukwa cha chiwerewere nakakwatira mkazi wina, achita chigololo.”
Ta intess tummu gays ba azinappe hara urara laymatonta dishin ba machcho anjidi hararo machcho ekizadey wuri laymates izikka gidees, anjetidarokka ekizadey izira laymates.
10 Ophunzira ake anati kwa Iye, “Ngati umu ndi mmene zilili pa mwamuna ndi mkazi, kuli bwino kusakwatira.”
Yesusa kalizayti izas machi wogayne azina wogay hayssamala gidikko machcho ekonta agoy lo7o gida.
11 Yesu anayankha kuti, “Si aliyense amene angavomere chiphunzitso ichi, koma kwa okhawo amene achimvetsetsa.
Gido atin Yesusay istas issi issi istas imetida asatappe atin hayssa timirteza onikka ekkanas danda7ena gidees.
12 Pakuti ena ndi akuti sangakwatire chifukwa anabadwa motero, ena ali motero chifukwa chofulidwa ndi anthu ndipo ena anawukana ukwati chifukwa cha ufumu wakumwamba. Iye amene angalandire ichi alandire.”
Gasoykka issi issi asay ba ayi uloppe yeletishe guddula gididi yeletes, issi issi asay asa kushen qaeatetidi gundilees, issi issi asay salo kawotethas gidi bena berka gudila othiza asikka dees. Haysa ekanas danda7izdey eekoo.
13 Pamenepo anabwera nawo ana kwa Yesu kuti awasanjike manja ndi kuwapempherera. Koma ophunzira ake anadzudzula amene anabweretsa anawo.
Qassekka yesusay ista bolla ba kushe wothidi wosana mala gutha nayta izakko ekki ehida gido attin iza kalizayti nayta ehida asata bolla hanqettida.
14 Yesu anati, “Lolani ana abwere kwa Ine, ndipo musawaletse pakuti ufumu wakumwamba ndi wa iwo onga anawa.”
Yesusay nayta ha taakko yero digofitee, salo kawotethi haytanta malasa gidees.
15 Atasanjika manja ake pa anawo, anachokapo.
Be kushe nayta bolla wothidi anjidappe guye heppe denddi bidees.
16 Taonani mnyamata wina anabwera kwa Yesu namufunsa kuti, “Aphunzitsi, ndi chinthu chiti chabwino chimene ndiyenera kuchita kuti ndipeze moyo wosatha?” (aiōnios )
Hessappe qasse issi uray Yesusakko shiqidi “tamarsizayso medhina de7o demanas demans ta lo7o otho ayi otho? gidi oychidees. (aiōnios )
17 Yesu anayankha kuti, “Ukundifunsiranji Ine za chinthu chimene ndi chabwino? Pali mmodzi yekha amene ndi wabwino. Ngati ukufuna kulowa mʼmoyo wosatha mvera malamulo.”
Yesusaykka tana aazas lo7o gish oychazi? Lo7oy isade xala, gede de7oy dizaso ne gelana koykko azazota naga gidees.
18 Mnyamatayo anamufunsa kuti, “Ndi ati?” Yesu anayankha kuti, “Usaphe, usachite chigololo, usabe, usapereke umboni onama,
Adezikka azazoti awayte? gidi oychidees. Yesusaykka zaridi “assi wodhoppa laymatoppa kaysotoppa wordo markatoppa ne awane ne ayo boncha ne shoro ne mala siqa gidees.
19 lemekeza abambo ako ndi amayi ako ndipo konda mnansi wako monga iwe mwini.”
20 Mnyamatayo anati, “Zonsezi ndimazisunga, nanga chatsala ndi chiyani?”
Wodalazikka zaridi hayssa ubbaa ta nagadis haray azi tas pacide? gidees.
21 Yesu anayankha kuti, “Ngati ukufuna kukhala wangwiro, pita kagulitse katundu wako ndi kupereka kwa osauka, ndipo udzakhala ndi chuma kumwamba. Ukakachita zimenezi, ukabwere udzanditsate Ine.”
Yesusaykka zaridi ne mule xilanakoykko bada ne haridaz ubbaa bayzada misha wursi manqotas imma neni salon mishe demandasa hessappe guye simma yada tana kala gidees.
22 Mnyamatayo atamva zimenezi, anachoka mokhumudwa, chifukwa anali ndi chuma chambiri.
Addezikka hessa siyidi izas daro mishi diza gish kehippe mishetishe bidees.
23 Pamenepo Yesu anati kwa ophunzira ake, “Zoonadi, ndikuwuzani kuti nʼkovuta kuti olemera akalowe mu ufumu wakumwamba.
Yesusaykka bena kalizata ta intes tumu gays dureti salo kawoteth gelaysi daro meto gidees.
24 Komanso ndikuwuzani kuti, nʼkwapafupi kuti ngamira idzere pa kabowo ka zingano kusiyana ndi kuti wolemera akalowe mu ufumu wa Mulungu.”
Qassekka ta intes gizay durey salo kawoteth gelanaysappe gamelay narfe lukora adhethi kawusha gida gidees.
25 Ophunzira atamva zimenezi, anadabwa kwambiri ndipo anamufunsa kuti, “Nanga angapulumuke ndani?”
Hessa siyida iza kalizayti dar qopidi histin oni atana danda7ize gidi Yesusa oychida.
26 Yesu anawayangʼana iwo nati, “Ndi anthu, izi nʼzosatheka, koma ndi Mulungu zinthu zonse zimatheka.”
Yesusaykka ista xelidi “haysi asa achan dandaetena Xoossa achan gidikko wurikka danda7etes gidees.
27 Petro anamuyankha Iye kuti, “Ife tinasiya zonse ndi kukutsatirani Inu! Nanga tsono ife tidzalandira chiyani?”
Phixirosaykka izas zaridi “nu nursikka agidi nena kalidos histin ha7i nu ayi demanesha gidees.
28 Yesu anawawuza kuti, “Zoonadi, ndikuwuzani kuti pa nthawi yokonzanso zinthu zonse, pamene Mwana wa Munthu adzakhala pa mpando wake waufumu mu ulemerero wake kumwamba, inu amene mwanditsata Ine mudzakhalanso pa mipando khumi ndi iwiri yaufumu, kuweruza mafuko khumi ndi awiri a Israeli.
Yesusaykka istas ta intess tumu gays asa nay buro yana oratha alamen ba boncho zupane bola utiza wode inte tan lakidayti tamane nam7u zupanne bola utidi tamane nam7u Isra7ele nayta bolla pirdana.
29 Ndipo aliyense amene wasiya nyumba, kapena abale, kapena alongo, kapena bambo kapena mayi kapena mkazi, kapena ana, kapena minda chifukwa cha Ine adzalandira madalitso ochuluka ndi kulandiranso moyo wosatha. (aiōnios )
Ta suntha gish gidi ba keth, ba ishata ba michista ba awane ba ayo ba nayta woykko ba bitta agiza assi wuri xetu kushe dikko ekkana medhina deyo latana. (aiōnios )
30 Koma ambiri amene ali oyambirira adzakhala omalizira, ndipo ambiri amene ndi omalizira adzakhala oyambirira.”
gido attin daro snthe gidida asati guye gidana, daro guyen diza asati sinthana.