< Mateyu 17 >
1 Patapita masiku asanu ndi limodzi Yesu anatenga Petro, Yakobo, ndi Yohane mʼbale wa Yakobo pa okha ndipo anakwera nawo pa phiri lalitali.
А через шість день забирає Ісус Петра, і Якова, і Івана, брата його, та й веде їх осі́бно на го́ру високу.
2 Pamenepo Iye anasinthika maonekedwe ake pamaso pawo. Nkhope yake inawala ngati dzuwa ndipo zovala zake zinayera kuti mbuu.
І Він перед ними переобрази́вся: обличчя Його, як те сонце, зася́ло, а одежа Його стала біла, як світло.
3 Nthawi yomweyo Mose ndi Eliya anaonekera kwa iwo akuyankhulana ndi Yesu.
І ось з'явились до них Мойсей та Ілля́, і розмовляли із Ним.
4 Petro anati kwa Yesu, “Ambuye ndi bwino kuti ife tikhale pano. Ngati mufuna ndidzamanga misasa itatu umodzi wanu, wina wa Mose ndi wina wa Eliya.”
І озвався Петро та й сказав до Ісуса: „Господи, до́бре бути нам тут! Коли хочеш, поста́влю оту́т три шатра: для Тебе одне, і одне для Мойсея, і одне для Іллі“.
5 Iye akuyankhulabe, mtambo owala unawaphimba, ndipo mawu ochokera mu mtambo anati, “Uyu ndiye Mwana wanga amene ndimukonda ndipo ndikondwera naye kwambiri. Mumumvere Iye!”
Як він ще говорив, ось хмара ясна заслони́ла їх, і ось голос із хмари почувсь, що казав: „Це Син Мій Улю́блений, що Його Я вподо́бав. Його слухайтеся!“
6 Ophunzira atamva zimenezi, anachita mantha nagwa pansi chafufumimba.
А почувши, попа́дали учні долі́лиць, і полякалися сильно.
7 Ndipo Yesu anabwera nawakhudza nati, “Dzukani, musaope.”
А Ісус підійшов, доторкнувся до них і промовив: „Уставайте й не бійтесь!“
8 Atayangʼana, sanaone wina aliyense kupatula Yesu yekha.
Звівши ж очі свої, ніко́го вони не побачили, окрім Само́го Ісуса.
9 Akutsika ku phiriko, Yesu anawalamula kuti, “Musawuze wina aliyense zimene mwaona, mpaka Mwana wa Munthu ataukitsidwa kwa akufa.”
А коли з гори схо́дили, заповів їм Ісус і сказав: „Не кажіть ніко́му про це виді́ння, аж поки Син Лю́дський із мертвих воскре́сне“.
10 Ophunzira anamufunsa Iye kuti, “Nanga nʼchifukwa chiyani aphunzitsi amalamulo amati Eliya ayenera kukhala woyamba kubwera?”
І запитали Його учні, говорячи: „Що́ це книжники кажуть, ніби треба Іллі́ перш прийти?“
11 Yesu anayankha kuti, “Kunena zoona, Eliya adzayenera kubwera ndipo adzakonza zinthu zonse.
А Він відповів і сказав: „Ілля́, правда, при́йде, і все приготу́є.
12 Koma Ine ndikuwuzani inu kuti Eliya anabwera kale koma iwo sanamuzindikire ndipo anachita naye chilichonse chimene anafuna. Momwemonso iwo adzazunza Mwana wa Munthu.”
Але́ кажу вам, що Ілля́ вже прийшов був, — та його не пізнали, але з ним зробили, що тільки хотіли. Так і Син Лю́дський має страждати від них“.
13 Pamenepo ophunzira anazindikira kuti amawawuza za Yohane Mʼbatizi.
Учні тоді зрозуміли, що Він їм говорив про Івана Христителя.
14 Atafika ku gulu la anthu, munthu wina anamuyandikira Yesu ndi kugwada pamaso pake.
І як вони до наро́ду прийшли, то до Нього один чоловік приступив, і навко́лішки впав перед Ним,
15 Iye anati, “Ambuye, muchitireni chifundo mwana wanga akudwala matenda akugwa ndipo akuvutika kwambiri. Kawirikawiri iye amagwa pa moto kapena mʼmadzi.
і сказав: „Господи, змилуйсь над сином моїм, що біснується у новомі́сяччі, і мучиться тяжко, бо почасту падає він ув огонь, і почасту в воду.
16 Ine ndinabwera naye kwa ophunzira anu koma alephera kumuchiritsa.”
Я його був привів до учнів Твоїх, — та вони не могли вздорови́ти його“.
17 Yesu anayankha nati, “Haa, mʼbado wosakhulupirira ndi wokhota maganizo! Kodi ndidzakhala nanu mpaka liti? Ndidzapirira nanu mpaka liti? Bwera nayeni kwa Ine mnyamatayo.”
А Ісус відповів і сказав: „О роде невірний і розбе́щений, доки бу́ду Я з вами? Доки вас Я терпітиму? Приведіть до Мене сюди його!“
18 Yesu anadzudzula chiwandacho ndipo chinatuluka mwa mnyamatayo ndipo anachira nthawi yomweyo.
Пото́му Ісус погрози́в йому, і де́мон вийшов із нього. І видужав хлопець тієї години!
19 Pamenepo ophunzira anabwera kwa Yesu mwamseri ndi kumufunsa kuti, “Chifukwa chiyani ife tinalephera kutulutsa chiwandacho?”
Тоді підійшли учні насамоті́ до Ісуса й сказали: „Чому ми́ не могли його вигнати?“
20 Iye anayankha kuti, “Chifukwa inu muli ndi chikhulupiriro chachingʼono. Zoonadi, Ine ndikuwuzani kuti ngati muli ndi chikhulupiriro monga kambewu ka mpiru, mukhoza kunena ndi phiri ili kuti, ‘Choka apa nupite apo,’ ndipo lidzachoka. Palibe kanthu kamene kadzakukanikani.
А Він їм відповів: „Через ваше невірство. Бо поправді кажу́ вам: коли будете ви мати віру, хоч як зе́рно гірчи́чне, і горі оцій скажете: „Перейди́ звідси туди“, то й пере́йде вона, і нічо́го не матимете неможливого!
21 Chiwanda cha mtundu uwu sichingachoke chabe koma ndi pemphero ndi kusala kudya.”
Цей же рід не вихо́дить інакше, як тільки молитвою й по́стом“.
22 Atasonkhana pamodzi ku Galileya, Iye anawawuza kuti, “Mwana wa Munthu akupita kukaperekedwa mʼmanja mwa anthu.
Коли пробува́ли вони в Галіле́ї, то сказав їм Ісус: „Людський Син буде ви́даний лю́дям до рук,
23 Iwo adzamupha koma pa tsiku lachitatu adzaukitsidwa.” Ndipo ophunzira anadzazidwa ndi chisoni.
і вони Його вб'ють, але третього дня Він воскре́сне“. І тяжко вони зажурились.
24 Yesu ndi ophunzira ake atafika ku Kaperenawo, wolandira msonkho wa ku Nyumba ya Mulungu anabwera kwa Petro namufunsa kuti, “Kodi aphunzitsi anu sapereka msonkho wa Nyumba ya Mulungu?”
Як прийшли ж вони в Капернау́м, до Петра підійшли збирачі́ дидра́хм на храм, та й сказали: „Чи не запла́тить ваш Учитель дидра́хми?“
25 Iye anayankha kuti, “Inde amapereka.” Petro atalowa mʼnyumba, Yesu ndiye anayamba kuyankhula. Ndipo anamufunsa kuti, “Ukuganiza bwanji Simoni, kodi mafumu a dziko lapansi amalandira msonkho kuchokera kwa ana awo kapena kwa ena?”
Він відказує: „Так“. І як він увійшов до дому, то Ісус попере́див його та сказав: „Як ти ду́маєш, Си́моне: царі зе́мні з кого беру́ть мито або пода́тки: від синів своїх, чи чужих?“
26 Petro anayankha kuti, “Kuchokera kwa ena.” Yesu ananena kwa iye kuti, “Ndiye kuti ana sapereka.”
А як той відказав: „Від чужих“, то промовив до нього Ісус: „Тож вільні сини!
27 Koma kuti ife tisawakhumudwitse pita ku nyanja kaponye mbedza yako. Katenge nsomba imene ukayambe kuyikola; kayitsekule kukamwa ndipo ukapezamo ndalama. Katenge ndalamayo ndi kukapereka msonkho wanga ndi wanu.
Та щоб їх не спокуси́ти, піди над море, та ву́дку закинь, і яку першу рибу ізло́виш, візьми, і рота відкрий їй, — і зна́йдеш стати́ра; візьми ти його, — і віддай їм за Мене й за себе“.