< Mateyu 16 >
1 Afarisi ndi Asaduki anabwera kwa Yesu ndi kumuyesa pomufunsa kuti awaonetse chizindikiro chochokera kumwamba.
Mafarisayo ni Masadukayo ikamuhanga ukamugema u Yesu alagiile ikilingasiilyo nikakupuma kilunde.
2 Iye anayankha kuti, “Kunja kukamada, inu mumati, kudzakhala nyengo yabwino popeza thambo ndi lofiira.
Kululo u Yesu akasusha akaaila, ang'wi impindi mukulunga singa iziza, kunsoko likoli ilunde ikauku.
3 Ndipo mmawa mumati, ‘Lero kudzakhala mvula yamphepo popeza thambo ndi lofiira ndi mitambo ya mvula.’ Inu mumadziwa kutanthauzira maonekedwe a thambo koma simungathe kutanthauzira zizindikiro za nthawi.
Ni kidaudau mukulunga ung'wega ileliye shanga uziza, migulya imalunde makauku du, kugoza ilingasilyo niamatungo shamumanyile.
4 Mʼbado woyipa ndi wachigololo umafuna chizindikiro chodabwitsa koma palibe ngakhale chimodzi chidzapatsidwa kupatula chizindikiro cha Yona.” Pamenepo Yesu anawasiya nachoka.
Wileli nuubi hangi nika ugoolya kikuduma kilingasiilyo, kutili kilingasilyo kihi nikikupegwa, iko iti du ni kang'wa Yona. Sunga u Yesu akaaleka akalongola.
5 Koma atawoloka nyanja, ophunzira anayiwala kutenga buledi.
I a manyingwa akiza inkigi akaabiia, akatula iwa shangaahoile imikate.
6 Yesu anawawuza kuti, “Chenjerani, khalani tcheru ndi yisiti wa Afarisi ndi Asaduki.”
U Yesu akaaila, tuli miho nuteele wa Mafarisayo nia Masadukayo.”
7 Iwo anakambirana pakati pawo za izi ndipo anati, “Ichi nʼchifukwa chakuti sitinatenge buledi aliyense.”
Iamanyisigwa akatulikolyo ienso nukulunga. Kunsoko shaaza kuhoile imikate.
8 Yesu atadziwa zokambirana zawo, anawafunsa kuti, “Chifukwa chiyani mukukambirana zakuti, ‘mulibe buledi?’ Inu achikhulupiriro chochepa.
U Yesu alilinga nilanso akaaila, unye nimukite uhuili nunino, niki nimasigo nukikolya unyenye, nukuhunga kina kunsoko shaaza muhoile imikate?
9 Kodi inu simukumvetsetsabe? Kodi simukukumbukira za buledi musanu amene anadya anthu 5,000 ndi madengu amene munadzaza?
Shamulingile ne hangi shamukimbukile imikate iyo mintaano kuantumagana anzogu muntaano, ni mbugulu inga naimuhoee?
10 Kapena buledi musanu ndi muwiri amene anadya anthu 4,000, nanga ndi madengu angati amene munadzaza?
Ang'wi mikate mupungate kuantu magana anzogu anne, ni mbugulu inga naimuhoile?
11 Zitheka bwanji kuti inu simukumvetsetsa kuti Ine sindinkayankhula nanu za buledi? Koma inu chenjerani ndi yisiti wa Afarisi ndi Asaduki.”
Yatulika uli kina shamulingile kina singa aikuligitya nunye kunsoko amikate? Igozi nuteele wa Mafarisayo ni Masadukayo.
12 Kenaka iwo anazindikira kuti Iye samawawuza kuti achenjere ndi yisiti wa buledi koma ndi chiphunzitso cha Afarisi ndi Asaduki.
Sunga ikalinga kina singa aukuaila ikie miho nimikate iyi nauteele, kina ihambe nuuteele wa Mafarisayo ni Masadukayo.
13 Yesu atafika ku chigawo cha Kaisareya Filipo, Iye anafunsa ophunzira ake kuti, “Kodi anthu amati Mwana wa Munthu ndi ndani?”
Matungo u Yesu naiwapika ku Kaisaria iyi na Filipi, akakolya lamanyisigwa akwe akazelunga antu akulunga ung'wana muntu iza nyenyu?
14 Iwo anayankha kuti, “Ena amati ndi Yohane Mʼbatizi; ena amati ndi Eliya; komanso ena amati Yeremiya kapena mmodzi wa aneneri.”
Ikalunga, niang'wi ilunga uyu Yohana Mbatizaji, niang'wi Eliya, niangiza Yeremia, niang'wi ang'wi anyakidagu.
15 Iye anafunsa kuti, “Nanga inuyo mumati ndine yani?”
Akaila unye milunga une ninyenyu?
16 Simoni Petro anayankha kuti, “Inu ndinu Khristu, Mwana wa Mulungu wamoyo.”
Simoni Petro akasusha, akalunga, “Ue ingi wi Kilisto ng'wana wang'wi Tunda numupanga.”
17 Yesu anati kwa iye, “Ndiwe wodala Simoni mwana wa Yona, popeza si munthu amene anakuwululira izi koma Atate anga akumwamba.
U Yesu akasusha akamuila, Bahu uewe Simoni Bar Yona. Kunsoko isakami numuili shangaikakulagiilaili. Ingi utata ne du nuakigulu.
18 Ndipo Ine ndikuwuza iwe kuti ndiwe Petro ndipo pa thanthwe ili Ine ndidzamangapo mpingo wanga ndipo makomo a ku gehena sadzawugonjetsa. (Hadēs )
Nene kuila uewe Petro numigulya nigwe iliite ukulizenga itekeelo lane. Ni moma nakuulungu shakulilemya. (Hadēs )
19 Ine ndidzakupatsa makiyi a Ufumu wakumwamba, ndipo chilichonse chimene iwe udzachimanga pansi pano chidzamangidwanso kumwamba.”
Kuupa iifungulo ya utemi wa kigulu, kihi nukukilugaila munkumbigulu, kikutula kalugailwa kigulu, hangi kihi iko nukukiluguila munkubigulu kikuluguilwa nukigulu.”
20 Pamenepo Iye anachenjeza ophunzira ake kuti asawuze wina aliyense kuti ndi Khristu.
Sunga u Yesu akaapa ilago iamanyisigwa aleke kumuila muntu wihi kina ng'wenso ai Kilisto.
21 Kuyambira nthawi imeneyo Yesu anayamba kuwafotokozera ophunzira ake kuti Iye ayenera kupita ku Yerusalemu ndi kukazunzidwa kwambiri mʼmanja mwa akulu a ansembe ndi aphunzitsi amalamulo kuti ayenera kuphedwa, ndi kuti tsiku lachitatu adzaukitsidwa.
Sunga imatungo yayo u Yesu akandya kuaila iamanyisigwa kina itulikile alongole ku Yerusalemu, winzagigwa ni nkani yidu, mumikono aanyampala nia kulu amakuhani niaika nkani, kubulagwa nukuuka uluhiku lakatatu.
22 Petro anamutengera Iye pambali nayamba kumudzudzula kuti, “Dzichitireni chifundo Ambuye, sizingachitike kwa Inu ayi.”
Sunga Petro akamuhola kumpelo akamkenela, akalunga, ulukani ulu lutule kule nuewe, “Mukulu ili lileke kupumila kitalako.
23 Yesu anatembenuka nati kwa Petro, “Choka pamaso panga Satana! Iwe ndi chokhumudwitsa kwa Ine; iwe suganizira zinthu za Mulungu koma zinthu za anthu.”
Ingi gwa u Yesu akapiluka akamuila Petro, “Suka kitalane mulugu uewe weenda ngilya kitalane, kunsoko shangaukee ulukani lang'wi Tunda, endu kee zizi niantu du.”
24 Pamenepo Yesu anati kwa ophunzira ake, “Ngati wina aliyense abwera pambuyo panga ayenera kudzikana ndi kutenga mtanda wake ndi kunditsata Ine.
Sunga u Yesu akaila iamanyisigwa akwe ang'wi muntu wihi nuloilwe kuntyata iime ihi namunkumbigulu, ahole uhuili wakwe, sunga antyate.
25 Pakuti aliyense amene afuna kupulumutsa moyo wake adzawutaya koma aliyense amene ataya moyo wake chifukwa cha Ine adzawupeza.
Uyu nuloilwe kuuguna upanga wa mihi ukulimilya, nuyu wihi kumalimilya kunsoko ane ukamaguna.
26 Kodi munthu adzapindula chiyani ngati atapeza zonse za dziko lapansi nataya moyo wake? Kapena munthu angapereke chiyani chosinthana ndi moyo wake?
Ukupata nsao ki umuntu aga amipate ihi hi kunu alimilye upanga wake? Kintu kii nukuila nuupanga wakwe?
27 Pakuti Mwana wa Munthu adzabwera mu ulemerero wa Atate ake ndi angelo ake ndipo pamenepo Iye adzapereka mphotho kwa munthu mofanana ndi zimene anachita.
Kululo ung'wana wang'wa Adamu uzile nuukulu wang'wa Tata akwe nia malaika akwe, ng'wenso uze apa ikinyamulimo iantu kukiila witumi wao.
28 “Ine ndikuwuzani inu choonadi, ena amene akuyimirira pano sadzalawa imfa asanaone Mwana wa Munthu akudza mu ufumu.”
Tai kumuila akoli apa ianyu niimikile singaaziza mionza insha sunga azizamuona ung'wa wang'wa Adamu nuzile muutemi wakwe.