< Mateyu 14 >
1 Pa nthawi imeneyo Mfumu Herode anamva za mbiri ya Yesu.
Che yo inako, Heroda munyandisi a zuwa za kavuvo ka Jesu.
2 Ndipo iye anati kwa antchito ake, “Uyu ndi Yohane Mʼbatizi; iye wauka kwa akufa! Ichi ndi chifukwa chake mphamvu zodabwitsa zikugwira ntchito mwa iye.”
Ni chawamba ku vahikana vakwe, cha ti, “U zu nji Joani Mukolovezi, a vakavuki kuvafwile. Ni hakuva vulyo aa maata a chikwete kuseveza kwali.”
3 Pakuti Herode anamugwira Yohane ndi kumumanga ndipo anamuyika mʼndende chifukwa cha Herodia mkazi wa mʼbale wake Filipo.
Chokuti Heroda a vakwete Joani, ni ku musumina, ni kumuvika muitolongo chevaka lya Herodiasi, muihabwe wa Filipi mwanche wakwe.
4 Chifukwa Yohane anakhala akunena kwa iye kuti, “Sichololedwa kwa inu kutenga mkaziyo.”
Chokuti Joani a vati kwali, “Kahena mulao kuti u ve naye nali mwihenu.”
5 Herode anafuna kupha Yohane koma iye anaopa anthu chifukwa anamuyesa iye mneneri.
Heroda ava kuswanela kumwihaya, kono a vatiyi vantu, chokuti va va kumuhinda kuti mupolofita.
6 Pa tsiku lokumbukira kubadwa kwa Herode, mwana wamkazi wa Herodia anavina pamaso pa anthu ndipo anasangalatsa kwambiri.
Kono izuva lya kupepwa kwa Heroda halisika, mwana wa Hedodiasi wa mukazana ava zani mukati mi chatavisa Heroda.
7 Kotero Herode analonjeza ndi lumbiro kumupatsa chilichonse chimene mwanayo angamupemphe.
Chakutava, cha sepisa cha kukonka kumuha chonse chete akumbile.
8 Ndipo atamupangira amayi ake anati, “Mundipatse pomwe pano mutu wa Yohane Mʼbatizi mʼmbale.”
Hamana kuhewa mulao kuvanyina, chati, “U nihe hahanu, mukasuva, mutwi wa Joani Mukolovezi.”.
9 Mfumuyo inamva chisoni koma chifukwa cha lumbiro lake ndi alendo amene anali pa phwando lake analamulira kuti chofuna chake chipatsidwe;
Simwine ni cha filikanywa hahulu chekupo yakwe, kono che vaka lya kukonka, ni chalivaka lya vo vavakulya naye, ni cha laula kuti kutendahale vulyo.
10 ndipo anakadula mutu wa Yohane mʼndende.
A ba tumini ni ku kakosala Joani mwintolongo.
11 Mutu wake anawubweretsa mʼmbale ndi kumupatsa mtsikanayo amene anawutengera kwa amayi ake.
Mi mutwi wakwe wa letwa mukasuva ni kuhewa ku mukazana mi cha utwalila va nyina.
12 Ophunzira a Yohane anabwera nadzatenga mtembo wake ndi kukawuyika mʼmanda. Pomwepo iwo anapita kukamuwuza Yesu.
Valutwana va kwe ni chivakeza, ni kuhinda chitupu, ni ku chizika. Ha vamana kuchita ezo, chi va yenda ku ka wambila Jesu.
13 Yesu atamva zimene zinachitika, anachoka pa bwato mwachinsinsi kupita kumalo a yekha. Magulu a anthu atamva izi anamutsatira Iye poyenda pansi kuchokera ku mizinda.
Hohwaho Jesu ha zuwa izo, a zwa muchivake echo ni chisepe ku ya kuchivaka chilikawile. Inyangela ha i zizuwa, chiya mwichilila chamatende kuzwa mwitolopo.
14 Yesu atafika ku mtunda, ndi kuona gulu lalikulu la anthu, Iye anamva nawo chifundo ndipo anachiritsa odwala awo.
Linu Jesu chakeza kubusu bwabo mi ni chabona inyangela. Cha vafwila mañeke ni ku hoza vakuli va vo.
15 Kutayamba mdima, ophunzira anabwera kwa Iye nati, “Kuno ndi kutchire ndipo kwayamba kale kuda. Awuzeni anthu azipita kuti afike ku midzi ndi kukadzigulira zakudya.”
Chiminemine chezuba ha chisika, valutiwa vakwe chi bekeza kwali chibati, “Chinu chibaka kachina vantu, mi izuva chilyemina. Hasanye inyangela, ilikuti bayende muminzi ni kukaliwulila zilyo.”
16 Yesu anawayankha kuti, “Sikofunika kuti azipita. Inuyo muwapatse kanthu kuti adye.”
Kono Jesu chawamba kuvali, “Kavena intuso ya kuya kule. Inwe muvahe chimwi chakulya.”
17 Iwo anayankha kuti, “Tili ndi malofu asanu okha a buledi ndi nsomba ziwiri.”
Chivati, “Twina hanu zinkwa bulyo zi kwanisa iyanza ni nswi zovele.”
18 Koma Iye anati, “Bweretsani kwa Ine.”
Jesu chati, “Muzilete kwangu.”
19 Analamula anthu kuti akhale pansi pa udzu ndipo anatenga buledi musanu ndi nsomba ziwiri nayangʼana kumwamba, nayamika nagawa bulediyo. Kenaka anapereka bulediyo kwa ophunzira ake ndipo ophunzirawo anagawira anthu.
Cwale Jesu a laula inyangela kuikala halyani. Chahinda zinkwa zi kwanisa iyanza ni nswi zovele. Na lolete kwiulu, chatoholofaza ni kucholola zinkwa ni kuziha valutwana. Valutwana chi vaziha inyangela.
20 Onse anadya nakhuta ndipo ophunzira anatola zotsalira ndi kudzaza madengu khumi ndi awiri.
Vavali ni kuikuta. Linu chibahinda vungululwa -vuvezuli zitanda zi na ikumi ni zobele.
21 Chiwerengero cha amene anadya kupatulako amayi ndi ana chinali pafupifupi amuna 5,000.
Vonse va valyi, va va kusaka kusika kuvakwame va zikiti zi zikwanisa iiyanza, kuzwisa vanakazi ni vahwile.
22 Nthawi yomweyo anawawuza ophunzira ake kuti alowe mʼbwato ndi kuti atsogole kupita kutsidya lina pamene Iye ankawuza anthu kuti azipita kwawo.
Hohwaho vulyo chawambila valutwana vakwe kukwela muchisepe balitangize kwali kwimwi mbali, mikuti iye mwine ha situmina inyangela kule.
23 Atatha kuwawuza kuti azipita kwawo, Iye anakwera ku phiri yekha kukapemphera. Pamene kumada anali kumeneko yekha.
Ha mana kuboza bungi bwabantu, chayenda heulu lyelundu yenke kukalapela. Linu chitengu ha chikolela a bena uko yenke.
24 Pamenepo nʼkuti bwato litapita patali pangʼono kuchokera ku mtunda ndipo linavutika ndi mafunde chifukwa mphepo inkawomba mokumana nalo.
Kono chisepe icho chi chivena hakati kewate, chi chivakupala kuyendiswa chevaka la mandinda, chokuti luhuho lu va kuchikanisa.
25 Pa ora lachinayi usiku, Yesu anabwera kwa iwo akuyendabe pa nyanja.
Mwinako ya bune ya masiku Jesu cha chuutila kubali, na yenda hewate.
26 Ophunzira atamuona akuyenda pa nyanja, anaopa nati, “Ndi mzukwa!” Ndipo analira chifukwa cha mantha.
Valutwana ha va muvona na yenda hewate, va vatiyi hahulu, ni chi bati, “Isaku,” mi chi vahuwa hahulu chakutiya.
27 Koma Yesu nthawi yomweyo anawawuza kuti, “Limbani mtima! Ndine, musaope.”
Kono Jesu cha wamba kuvali haho ni chati, “Mukole! Njeme! Kanji mutiyi.”
28 Petro anayankha nati, “Ambuye ngati ndinu, mundiwuze ndibwere kuli inuko pa madzipo.”
Pitorosi cha mwitava chati, “Simwine, haiva nje we, ni laele ni niize kwako hamenzi.
29 Iye anati, “Bwera.” Pamenepo Petro anatuluka mʼbwato ndipo anayenda pa madzi kupita kwa Yesu.
Jesu chati, “Wize.” Cwale Pitorosi cha suka muchisepe ni kuyenda ha menzi kuya kwa Jesu.
30 Koma ataona mphepo, iye anachita mantha ndipo anayamba kumira, nafuwula nati, “Ambuye ndipulumutseni!”
Kono Pitorosi ha vona luhuho, chatiya. Hakalisa bulyo kumina, cha huwa ahulu chati, “Simwine, nihaze!”
31 Ndipo mofulumira Yesu anatambasula dzanja lake namugwira iye, nati, “Iwe wachikhulupiriro chochepa, bwanji unakayika?”
Jesu haho vulyo cha otolola iyanza lyakwe, cha kwata Pitorosi, mi ni chamulwila kuti, “Iwe we ntumelo inini, chinzi hohonona?”
32 Ndipo atalowa mʼbwato mphepo inaleka.
Linu cwale Jesu ni Pitorosi chiba yenda muchisepe, luhuho chilwa siya kuhunga.
33 Pamenepo amene anali mʼbwato anamulambira Iye, nati, “Zoonadi, Inu ndinu Mwana wa Mulungu.”
Cwale valutwana muchisepe chiva lapela Jesu chibati, “Cheniti u Mwana Mulimu.”
34 Atawoloka, anafika ku Genesareti.
Ha chiva lutite, chi venjila munkanda ya Genezareta.
35 Anthu akumeneko atamuzindikira Yesu, iwo anatumiza mawu kwa onse ozungulira deralo. Anthu anabwera ndi odwala awo onse kwa Iye.
Linu vantu mwechina chibaka chivalemuha Jesu, chivatumina mañusa monse muzivaka zimbulukite chilalanda, mi chivamuletela vonse vavakulwala.
36 Ndipo anamupempha alole kuti akhudze mphonje ya mkanjo wake, ndipo onse amene anamukhudza anachiritsidwa.
Chibamukumbila kuti vakwate vulyo kumungundo we chizwato chakwe, mi vungi vu vakwati kwateni chibwahola.