< Mateyu 12 >
1 Pa nthawi imeneyo Yesu anadutsa pakati pa minda ya tirigu pa tsiku la Sabata. Ophunzira ake anamva njala nayamba kuthyola ngala za tirigu nʼkumadya.
Omwanya ogwo Yesu agendele kulusiku lwa isabhato alabhile mumabwi. Abheigisibhwa bhae bhaliga bhalumilwe omweko nibhamba okufuna ebhyangala nokulya.
2 Afarisi ataona zimenezi anati kwa Iye, “Taonani! Ophunzira anu akuchita zosaloledwa pa tsiku la Sabata.”
Nawe Amafalisayo bhejile okulola kutyo, nibhamubhwila ati Yesu “Lola abheigisibhwa bhao kutyo abhatambuka ebhilagilo abhakola jinu jiteile olusiku lwa Isabhato”
3 Iye anayankha kuti, “Kodi simunawerenge zimene anachita Davide pamene iye ndi anzake anamva njala?
Nawe Yesu nabhabhwila ati, “Mchali kusoma kutyo Daudi akolele, omwanya gunu alumilwe omweko, amwi na bhanu bhanu aligaalinabho?
4 Analowa mʼNyumba ya Mulungu, ndipo iye ndi anzakewo anadya buledi wopatulika amene sikunali kololedwa kwa iwo kudya koma ansembe okha.
Lwakutyo engiye munyumba ya Nyamuanga nalya emikate ja bhagabhisi, jinu jaliga jitamwiile omwene okujilya na bhanu aliga anabho, na kutyo jaliga jiile ku Bhagabhisi?
5 Kodi simunawerenge mʼmalamulo kuti pa Sabata ansembe mʼNyumba ya Mulungu amaphwanya lamulo la Sabata komabe sawayesa olakwa?
Muchali kusoma mubhilagilo ati, kulusiku lwa Isabhato abhagabhisi munda ya iyekalu abhaikaya Isabhato, nawe bhatana chikayo?
6 Ine ndikuwuzani kuti wamkulu kuposa Nyumba ya Mulunguyo ali pano.
Nawe enaika kwemwe ati, unu alimukulu okukila liyekalu alyanu.
7 Ngati mukanadziwa zomwe mawu awa atanthauza, ‘Ine ndifuna chifundo osati nsembe,’ inu simukanatsutsa osalakwa.
Mwakabhee nimumenya inu obhugajulo bhwayo niki, enenda echigongo ntakwenda echitambo; mutakabhalamuye bhanu bhatana ntambala,
8 Pakuti Mwana wa Munthu ndiye Mbuye wa Sabata.”
Kulwokubha Omwana wa Adamu nuwe Omukama wa Isabhato.”
9 Atachoka kumeneko anakalowa mʼsunagoge mwawo.
Neya Yesu nasokao nagenda mulikofyanyisho lyebhwe.
10 Ndipo mʼmenemo munali munthu wolumala dzanja. Pofuna chifukwa chokamunenezera, iwo anamufunsa Yesu kuti, “Kodi nʼkololedwa kuchiritsa munthu tsiku la Sabata?”
Lola aliga alio omunu aliga afuye okubhoko. Amafalisayo nigamubhusha Yesu, nibhamubhusha ati, “Enibhusha jiile okwiulisha olusiku lwa Isabhato?” koleleki bhabhone okumusitaka kwo kukola ebhibhibhi.
11 Iye anawawuza kuti, “Ngati wina wa inu ali ndi nkhosa nigwera mʼdzenje tsiku la Sabata, kodi simudzayigwira ndi kuyitulutsa kunja?
Yesu nabhabhwila ati, “Niga umwi mwimwe, unu kabha ali na inyabhalega imwi, na inyabhalega eyo nigwa mulyobho olusiku lwa Isabhato, mutamugwata kwa managa mumusosha mulyobho?
12 Nanga munthu sali oposa nkhosa kwambiri! Chifukwa chake nʼkololedwa kuchita zabwino pa Sabata.”
Enibhusha niki chinu echainsonga, okukila, itali okukila inyabhalega! Kulwejo jiile okukola ejakisi kulusiku lwa Isabhato.”
13 Pamenepo Yesu anati kwa munthuyo, “Wongola dzanja lako.” Iye analiwongola ndipo linakhala monga linalili kale.
Neya Yesu namubhwila omunu oyo ati, “Golola okubhoko kwao” Nakugolola, nikubhona nikwiulila, lwo kundi.
14 Koma Afarisi anatuluka kunja ndi kukonza njira yoti amuphere.
Nawe Amafalisayo nibhauluka anja nibhakola echenge echokwenda okumusimagisha nibhagenda anja okuloma bhatasikene nage. Bhaliga nibhayenja okumwita.
15 Podziwa zimenezi, Yesu anachoka kumalo amenewo. Ambiri anamutsata Iye ndipo anachiritsira odwala awo onse
Yesu ejile amenya elyo nasokao awo. Bhanu bhamfu nibhamulubha, nabhaosha bhona.
16 nawachenjeza kuti asamuwulule kuti yani.
Nabhalagilila bhataja kumukola akamenyekana kubhandi,
17 Uku kunali kukwaniritsa zimene zinayankhulidwa kudzera mwa mneneri Yesaya kuti,
koleleki chikumile echimali, chinu chaliga chaikilwe no mulagi Isaya, naikati,
18 “Taonani mnyamata wanga amene ndinamusankha, Wokondedwa wanga, amene moyo wanga ukondwera naye. Pa Iye ndidzayika Mzimu wanga, ndipo Iye adzalalikira chiweruzo kwa akunja.
Lola, omukosi wani unu nauye, omwedwa wani, kumwene omwoyo gwani ogukondelelwa. Nilita Omwoyo gwani ingulu yae, na kalasha indamu Kubhanyamaanga.
19 Sadzalimbana, sadzafuwula, ngakhale mmodzi sadzamva mawu ake mʼmakwalala.
Atakunyanka nolo kulila kwa managa; atalio munu alyugwa obhulaka bhwae munjila.
20 Bango lophwanyika sadzalithyola, ndi nyale yofuka sadzayizimitsa, kufikira Iye adzatumiza chiweruziro chikagonjetse.
Atalilifuna lisaunga linu lyatikile; atalisimya lutambi lwona lwona lunu olwituta ingesi, okukinga anu aliletela indamu yo bhusingi.
21 Ndipo akunja adzakhulupirira dzina lake.”
Amaanga galibha nobhuigi kwisina lyae.
22 Pomwepo anthu anabwera naye kwa Yesu munthu wogwidwa ndi chiwanda amene anali wosaona ndi wosamva ndipo Yesu anamuchiritsa kotero kuti atatha anayamba kumva ndi kuona.
Omunu umwi aliga alimuofu na ali mutita, unu aliga agwatwilwe na masabhwa naletwa imbele ya Yesu. Namuosha, amwi lwakutyo aliga ali mutita alomele no kulola.
23 Anthu onse anadabwa ndipo anati, “Kodi uyu ndi kukhala mwana wa Davide?”
Liijo lyona nililugula nilyaikati, “Lugendo omunu unu niwe omwana wa Daudi?”
24 Koma Afarisi atamva zimenezi, anati, “Uyu amatulutsa ziwanda ndi mphamvu ya Belezebabu mkulu wa ziwandazo.”
Nawe omwanya gunu Abhafalisayo bhejile bhongwa echilugusho echo, nibhaikati, “Omunu unu atakusoshako amasabhwa kwa managa gae tali kumanaga ga Belzebuli, omukulu wa masabhwa.
25 Yesu anadziwa maganizo awo ndipo anawawuza kuti, “Ufumu uliwonse ukagawanika mwa iwo udzawonongeka ndi mzinda uliwonse kapena banja likagawanika, mwa izo zokha sizidzayima.
“Nawe Yesu namenya obhiganilisha bhwebhwe nabhabhwila ati,”Bhuli bhukama bhunu bhugabhanyikile obhwene obhunyamuka, na bhuli musi amwi bhuli nyumba inu eigabhanyika eyene itakusimbagilila.
26 Ngati Satana atulutsa Satana, iye adzigawa yekha. Nanga ufumu wake ungayime bwanji?
Ikabha Shetani, namusoshako Shetani, menya kebhuma omwene,
27 Ndipo ngati Ine nditulutsa ziwanda ndi Belezebule, anthu anu amatulutsa ziwandazo ndi chiyani? Potero tsono adzakhala oweruza anu.
Nikutiki obhukama bhwae obhwimelegulu? Akasoshako amasabwa kwa managa ga Belizabuli, abhaemba bhemwe abhagasoshako kwa njila yaga? Kwo kulubha linu bhalibha bhalamusi bhemwe.
28 Koma ngati Ine ndimatulutsa ziwanda ndi Mzimu wa Mulungu, pamenepo ufumu wa Mulungu wafika pa inu.
Na labha enisoshako amasabwa kwa managa go Mwoyo gwa Nyamuanga, mumenye ati obhukama bhwa Nyamuanga bhwaja kwimwe.
29 “Kapenanso wina aliyense angathe bwanji kulowa mʼnyumba ya munthu wamphamvu ndi kunyamulamo zinthu zake, sipokhapo atayamba wamanga munthu wa mphamvuyo? Pamenepo iye akhoza kuba mʼnyumbamo.
No munu katula atiki okwingila munyumba yo munu wa managa nokwibha, bila kumubhoya owamanaga okwamba? Niwo kebha ebhinu bhyae okusoka munyumba ya.
30 “Iye amene sali ndi Ine atsutsana nane ndipo iye amene sasonkhanitsa pamodzi ndi Ine amamwaza.
Wona wona unu atali amwi nanye chitasikene, na unu atakukumanya amwi nanye oyo kanyalambula.
31 Ndipo potero Ine ndikuwuzani inu, tchimo lililonse ndi cha mwano chilichonse zidzakhululukidwa kwa anthu koma chamwano cha pa Mzimu Woyera, sichidzakhululukidwa.
Kulwejo enaika kwimwe, bhuli chibhibhi no kugaya abhanu bhalisasilwa, tali okumugaya Omwoyo Mwelu bhatalisasilwa.
32 Aliyense amene anena mawu otsutsana ndi Mwana wa Munthu adzakhululukidwa koma aliyense wonena motsutsana ndi Mzimu Woyera sadzakhululukidwa mu mʼbado uno kapena umene ukubwerawo. (aiōn )
Na wona wona alyaika omusango kutasikene no Mwana wa Adamu, elyo alisasilwa. Nawe unu alyaika atasikene no Mwoyo Mwelu, oyo atalisasilwa, muchalo munu, nolo bhunu bhulija. (aiōn )
33 “Mtengo wabwino umabala zipatso zabwino ndipo mtengo woyipa umabalanso zipatso zoyipa, pajatu mtengo umadziwika ndi zipatso zake.
Amo ukole liti okubha lyekisi na matwasho galyo gakisi, amo unyamule liti na matwasho galyo, kulwokubha liti elimenyekana kwa matwasho galyo.
34 Ana anjoka inu, woyipa inu, mungathe bwanji kuyankhula kanthu kalikonse kabwino? Pakuti pakamwa pamayankhula zosefuka kuchokera mu mtima.
Emwe olwibhulo lwa injoka, emwe muli bhabhibhi, omutula atiki okwaika emisango jakisi? Kulwokubha omunwa oguloma ganu agasoka mumwoyo.
35 Munthu wabwino amatulutsa zinthu zabwino zomwe zili mumtima mwake ndipo munthu woyipa amatulutsanso zinthu zoyipa zomwe zili mwa iye.
Omunu wo bhwana mwibhikilo lyo mwoyo gwae agasokamo agobhwana, no munu omubhibhi mwibhikilo lyae elyobhunyamuke, echisokamo echibhibhi.
36 Ine ndikukuwuzani kuti pa tsiku la chiweruziro munthu adzazengedwa mlandu chifukwa cha mawu aliwonse wopanda pake amene anayankhula.
Enibhabhwila ati kulusiku lwa indamu abhanu bhalisosha olubhala lwa bhuli musango gwo bhwana gunu bhaikile.
37 Pakuti ndi mawu anu mudzapezeka osalakwa ndiponso ndi mawu anu mudzapezeka olakwa.”
Kulwokubha kwe misango jao oubhalilwa obhulengelesi na kwemisango jao oulamulwa.”
38 Pamenepo ena mwa Afarisi ndi aphunzitsi amalamulo anati kwa Iye, “Aphunzitsi, tikufuna tione chizindikiro chodabwitsa kuchokera kwa Inu.”
Nibheya agati ya bhandiki na Mafalisayo nibhamusubhya Yesu nibhaikati, “Mwiigisha, echenda okulola echilugusho okusoka kwawe.”
39 Iye anayankha kuti, “Mʼbado woyipa ndi wachigololo ufunsa za chizindikiro chodabwitsa! Koma ndi chimodzi chomwe sichidzapatsidwa kwa inu kupatula chizindikiro cha mneneri Yona.
Nawe Yesu nasubhya naikati,” Olwibhulo olujabhi olwobhusiani, echenda echilugusho. Nawe chitalio chilugusho chinu chilisosibhwa tali echilugusho cha Yona omulagi.
40 Pakuti monga Yona anali mʼmimba mwa nsomba yayikulu masiku atatu, usana ndi usiku, momwemonso Mwana wa Munthu adzakhala masiku atatu, usana ndi usiku, mʼkati mwa nthaka.
Na lwakutyo omulagi Yona ekae munda ya inswi nene kwo mwanya gwa nsiku esatu mumwisi na mungeta, kutyo nikwo Omwana wa Adamu alibha munda yo mwoyo gwa inside nsiku esatu mumwisi na mungeta.
41 Anthu a ku Ninive adzayimirira pachiweruzo ndi mʼbado uwu ndi kuwutsutsa pakuti iwo analapa Yona atalalikira ndipo tsopano wamkulu kuposa Yona ali pano.
Abhanu bha Ninawi bhalimelegulu imbele ya indamu amwi nolwibhulo lwa bhanu bhanu na bhalichilamula. Kulwokubha bhatee kwo kulasha kwa Yona, lola, omunu umwi mukulu okukila Yona alyanu.
42 Mfumu yayikazi yakummwera idzayimirira pa tsiku lachiweruzo ndi mʼbado uwu ndipo idzawutsutsa pakuti inachokera kumathero a dziko lapansi kudzamva nzeru za Solomoni, ndipo pano pali woposa Solomoni.
Omukama omugasi owamumalimbe alimuka mundamu amwi na bhanu bho lwibhulo lunu nalulamula. Ejile okusoka kubhutelo bhwe chalo naja okungwa obhwengeso bwa Selemani, Lola, omunu umwi okukila Selemani alyanu.
43 “Pamene mzimu woyipa utuluka mwa munthu, umadutsa malo wopanda madzi kufunafuna malo opumulira ndipo suwapeza.
Omwanya gunu lisabhwa libhibhi elimusokako omunu, elilabha anu gatali manji ndiyenja owokuumula, nawe litakubhona
44 Pamenepo umati, ‘Ndidzabwerera ku nyumba yanga komwe ndinatuluka.’ Pamene ufika, upeza mopanda kanthu, mosesedwa ndi mokonzedwa bwino.
Eliiya nilyaikati, 'enisubha munyumba yani inu nisokekelemo. 'Likasubha ndisanga inyumba ikukumbile imaliliye.
45 Kenaka umapita kukatenga mizimu ina isanu ndi iwiri yoyipa kwambiri kuposa uwowo ndipo imapita ndi kukakhala mʼmenemo. Choncho khalidwe lotsiriza la munthu uyu limakhala loyipa kwambiri kuposa loyambalo. Umo ndi mmene zidzakhalire ndi mʼbado oyipawu.”
Eligenda ndileta agandi amasabhwa Saba ganu galimabhibhi okukila elyo, nigekalao gona. No bhutulo obhubha bhubhibhi okukila obhwokwamba. Kutyo nikwo jilibha kulwibhulo lunu olunyamuke.
46 Pamene Yesu anali kuyankhulabe ndi gulu la anthu, amayi ndi abale ake anayimirira kunja, akufuna kuyankhulana naye.
Omwanya gunu Yesu aliga naloma na liijo lola, nyilamwene na bhamula bhabhwo bhemeleguyu anja, nibhendaga okuloma nage.
47 Wina anamuwuza Iye kuti, “Amayi ndi abale anu ayima kunjaku akufuna kuyankhulana nanu.”
Omunu umwi namubhwila ati,”Lola nyokomwana na bhamula bhanyu bhalianja, abhenda okuloma nawe.”
48 Iye anayankha kuti, “Amayi anga ndani ndipo abale anga ndi ndani?”
Nawe Yesu namusubhya unu ejile okumubhwila,”Mayi wani niga? na bhamula bhasu nibhaga?”
49 Ndipo akuloza ophunzira ake, Iye anati, “Awa ndiwo amayi anga ndi abale anga.
Nasomelesha ku bheigisibhwa bhae naikati,”Lola, bhanu nibho bhamayi na bhamula bhasu!
50 Pakuti aliyense amene achita chifuniro cha Atate anga akumwamba ndiye mʼbale wanga, mlongo wanga ndi amayi anga.”
Kulwokubha wona wona unu kakola ebhyo Rata wani wa mulwile kenda, omunu oyo niwe omula wasu, omuyala wasu na mayi wani.”