< Mateyu 12 >

1 Pa nthawi imeneyo Yesu anadutsa pakati pa minda ya tirigu pa tsiku la Sabata. Ophunzira ake anamva njala nayamba kuthyola ngala za tirigu nʼkumadya.
Hesappe guye Yesusay sambata galas kaththa gidora adhi bidess. Iza kalizaytikka gafida gish tiya duthidi shigechi muus oykidda.
2 Afarisi ataona zimenezi anati kwa Iye, “Taonani! Ophunzira anu akuchita zosaloledwa pa tsiku la Sabata.”
Parisaweti hessa beyidi Yesusa “hekko nena kalizayti sambata galas oothistanas besontaysa oothetess gidda.”
3 Iye anayankha kuti, “Kodi simunawerenge zimene anachita Davide pamene iye ndi anzake anamva njala?
Izikka istas zaridi “Dawiteyinne izara diza asati gafida wode izi ay othidakkone nababibeyketi?
4 Analowa mʼNyumba ya Mulungu, ndipo iye ndi anzakewo anadya buledi wopatulika amene sikunali kololedwa kwa iwo kudya koma ansembe okha.
Xoossa keth gelidi qesistappe attin Dawiteyne izara dizayti bochanas besonta dumma uketh midess.
5 Kodi simunawerenge mʼmalamulo kuti pa Sabata ansembe mʼNyumba ya Mulungu amaphwanya lamulo la Sabata komabe sawayesa olakwa?
Woykko qeseti sambata sharidi meqidess gidon otho othikko moro gidontaysa ooritte wogappe nababibeyketi?
6 Ine ndikuwuzani kuti wamkulu kuposa Nyumba ya Mulunguyo ali pano.
Gidikkokka ta intess gizay meqdeseppe adhizadey han dess.
7 Ngati mukanadziwa zomwe mawu awa atanthauza, ‘Ine ndifuna chifundo osati nsembe,’ inu simukanatsutsa osalakwa.
“Yarsho gidonta ta maroteth dosays” giza qaalay ay gusukunne inte erizakko xillota bolla pirdekistakkoshin
8 Pakuti Mwana wa Munthu ndiye Mbuye wa Sabata.”
asa nay sanbatas godda” gidees.
9 Atachoka kumeneko anakalowa mʼsunagoge mwawo.
Heppe izi gede adhishe ista mukurabe gelidess.
10 Ndipo mʼmenemo munali munthu wolumala dzanja. Pofuna chifukwa chokamunenezera, iwo anamufunsa Yesu kuti, “Kodi nʼkololedwa kuchiritsa munthu tsiku la Sabata?”
Henikka issi kushe silidadey dess. Yesuusa kasasanas gasso koyidi “sambata galas pathanas besize?” gidi iza oychidess.
11 Iye anawawuza kuti, “Ngati wina wa inu ali ndi nkhosa nigwera mʼdzenje tsiku la Sabata, kodi simudzayigwira ndi kuyitulutsa kunja?
Izikka ista “inteppe isadde dorsi sambata galas olan gilikko ba dorssa izi gelidi ollafe gochi kessi erene?
12 Nanga munthu sali oposa nkhosa kwambiri! Chifukwa chake nʼkololedwa kuchita zabwino pa Sabata.”
Histikko assi dorssappe kehi adhene? hessa gish sambata galas lo7o oothoy digetena” gidess.
13 Pamenepo Yesu anati kwa munthuyo, “Wongola dzanja lako.” Iye analiwongola ndipo linakhala monga linalili kale.
Addeza “ne kushe pidisa” gidess, addezikka ba kushe pidisin hinkko kusheza mala paxa gididees.
14 Koma Afarisi anatuluka kunja ndi kukonza njira yoti amuphere.
Giddo atin parsaweti heppe kezidine Yesuusa wosti oyki wodhanakone ba garsan zoretidda.
15 Podziwa zimenezi, Yesu anachoka kumalo amenewo. Ambiri anamutsata Iye ndipo anachiritsira odwala awo onse
Yesusay ista qohaaththaa eridi heppe haraso deesh gidess. Daro derey iza kalidess harganchatakka wursi pathidess.
16 nawachenjeza kuti asamuwulule kuti yani.
Izi onakone asas yotonta mala ista azazidess.
17 Uku kunali kukwaniritsa zimene zinayankhulidwa kudzera mwa mneneri Yesaya kuti,
Hesikka haniday nabe Isayasan “Ta doridayne ta izan ufa7etiza ta nay haysich; ta ayanappe ta iza bolla wothana, izikka amanonta deretas tumu pirda awajana, oyetena, woykko wassena. Izas qalaykka karen siyetena, Tuma pirda xonos gathana gakanas tinceti utida shomboqokka menthenane cuwatiza muqadakka toysena, amanonta dereti iza ufaysan nagana” getetidi yotetida tinbite qalay polistana.
18 “Taonani mnyamata wanga amene ndinamusankha, Wokondedwa wanga, amene moyo wanga ukondwera naye. Pa Iye ndidzayika Mzimu wanga, ndipo Iye adzalalikira chiweruzo kwa akunja.
19 Sadzalimbana, sadzafuwula, ngakhale mmodzi sadzamva mawu ake mʼmakwalala.
20 Bango lophwanyika sadzalithyola, ndi nyale yofuka sadzayizimitsa, kufikira Iye adzatumiza chiweruziro chikagonjetse.
21 Ndipo akunja adzakhulupirira dzina lake.”
22 Pomwepo anthu anabwera naye kwa Yesu munthu wogwidwa ndi chiwanda amene anali wosaona ndi wosamva ndipo Yesu anamuchiritsa kotero kuti atatha anayamba kumva ndi kuona.
Hessappe guye daydanthi oykin xelanasine hasa7anas dayda7onta issi ura Yesusakko ekki yida. Yesusaykka iza pathin addezi xelanassine hasa7anas dandaydess.
23 Anthu onse anadabwa ndipo anati, “Kodi uyu ndi kukhala mwana wa Davide?”
Assay wurikka malaletidi “haysi addezi Dawite nasha?” gidess.
24 Koma Afarisi atamva zimenezi, anati, “Uyu amatulutsa ziwanda ndi mphamvu ya Belezebabu mkulu wa ziwandazo.”
Giddo atin parsaweti hessa siyda wode “Haysi addezi daydanth kesizay daydantha halaqa bi7el zebula wolqan xala gidanas besses” gida.
25 Yesu anadziwa maganizo awo ndipo anawawuza kuti, “Ufumu uliwonse ukagawanika mwa iwo udzawonongeka ndi mzinda uliwonse kapena banja likagawanika, mwa izo zokha sizidzayima.
Yesusay ista qofa eridi “ba garsan isay issappe shaketiza kawotethi wurikka kundana, ba garsan shaketiza katamay woykko ketha assi minena.
26 Ngati Satana atulutsa Satana, iye adzigawa yekha. Nanga ufumu wake ungayime bwanji?
Xala7ey Xala7e kesiza gidkko Xala7ey ba garasan shaketidess gusa. Hessatho hanikko iza kawotethi wani minana danda7ize?
27 Ndipo ngati Ine nditulutsa ziwanda ndi Belezebule, anthu anu amatulutsa ziwandazo ndi chiyani? Potero tsono adzakhala oweruza anu.
Tani bi7el zebula wolqan kesiza gidikko inte nayti aza woliqan kesane? Hessa gish inte nayti inte bolla pirdana.
28 Koma ngati Ine ndimatulutsa ziwanda ndi Mzimu wa Mulungu, pamenepo ufumu wa Mulungu wafika pa inu.
Gido atin tani daydanth kesizay Xoossa ayanan gidikko Xoossa kawotethi intekko yidess gussa.
29 “Kapenanso wina aliyense angathe bwanji kulowa mʼnyumba ya munthu wamphamvu ndi kunyamulamo zinthu zake, sipokhapo atayamba wamanga munthu wa mphamvuyo? Pamenepo iye akhoza kuba mʼnyumbamo.
Woykko issi uray wolqara dizade keth gelidi mishe bonqana koyikko kasetidi he wolqara dizadeza oyki qashonta wosti bonqane? Qachidappe guye bonqana dandayes.
30 “Iye amene sali ndi Ine atsutsana nane ndipo iye amene sasonkhanitsa pamodzi ndi Ine amamwaza.
Tanara gidontadey tanara eqetes, tanara issippe shishonta uray wurikka lales.
31 Ndipo potero Ine ndikuwuzani inu, tchimo lililonse ndi cha mwano chilichonse zidzakhululukidwa kwa anthu koma chamwano cha pa Mzimu Woyera, sichidzakhululukidwa.
Hessa gish ta intess tumu gays nagara othoyne cashi wuri asas ato getistana shin Xillo ayana cayida uray maretena.
32 Aliyense amene anena mawu otsutsana ndi Mwana wa Munthu adzakhululukidwa koma aliyense wonena motsutsana ndi Mzimu Woyera sadzakhululukidwa mu mʼbado uno kapena umene ukubwerawo. (aiōn g165)
Ay assikka asa na bolla hasa7iza iitta qaalay maristana shin Xillo Ayana bolla hasa7iza iita qaalay gidikko hayssa ha woden gidin woykko buro yana woden gidin maroy deena. (aiōn g165)
33 “Mtengo wabwino umabala zipatso zabwino ndipo mtengo woyipa umabalanso zipatso zoyipa, pajatu mtengo umadziwika ndi zipatso zake.
Mithi wuri ayfen eretizaysa mala inte lo7o ayfe demana mala intes lo7o mithi deyo, intes iita mithi diza gidikko inte ita ayfe ekkana.
34 Ana anjoka inu, woyipa inu, mungathe bwanji kuyankhula kanthu kalikonse kabwino? Pakuti pakamwa pamayankhula zosefuka kuchokera mu mtima.
Inteno marzera diza shoshato inteni iitata gidi utidi wosti lo7o hasa7anas dandayeti? Ulo garsan kumidazi dunara hasa7etess.
35 Munthu wabwino amatulutsa zinthu zabwino zomwe zili mumtima mwake ndipo munthu woyipa amatulutsanso zinthu zoyipa zomwe zili mwa iye.
Lo7o assi ba wozinan kunthi wothida lo7o yooppe lo7o hasa7es, iitta assikka ba wozinan kunthi wothidda itatethappe iitta yo kesses.
36 Ine ndikukuwuzani kuti pa tsiku la chiweruziro munthu adzazengedwa mlandu chifukwa cha mawu aliwonse wopanda pake amene anayankhula.
Gido atin ta intess gizay asay ba hasa7ida hada qaala wurso gish pirda galas wurikka oychistana.
37 Pakuti ndi mawu anu mudzapezeka osalakwa ndiponso ndi mawu anu mudzapezeka olakwa.”
Gassoykka ne qalappe dendidaysan ne xilada atanane ne qalappe dendidaysan ne bolla pirdistana
38 Pamenepo ena mwa Afarisi ndi aphunzitsi amalamulo anati kwa Iye, “Aphunzitsi, tikufuna tione chizindikiro chodabwitsa kuchokera kwa Inu.”
Hessappe guye issi issi Musse woga tamarsizaytine parsaweti Yesusa “astamare, nu neppe malalsiza malata beyanas koyos” gida.
39 Iye anayankha kuti, “Mʼbado woyipa ndi wachigololo ufunsa za chizindikiro chodabwitsa! Koma ndi chimodzi chomwe sichidzapatsidwa kwa inu kupatula chizindikiro cha mneneri Yona.
Izi istass zaridi “ha iitane layma yeletay malata oyches gido attin nabbe Yoonasa malatappe atin hara malatay imetena” gidess.
40 Pakuti monga Yona anali mʼmimba mwa nsomba yayikulu masiku atatu, usana ndi usiku, momwemonso Mwana wa Munthu adzakhala masiku atatu, usana ndi usiku, mʼkati mwa nthaka.
Yoonasay gita mole ulo giidon heedzdzu qamane hezu galas gami7ida mala asa nay hezu galasine hezu qamma bitta ulon gam7ana.
41 Anthu a ku Ninive adzayimirira pachiweruzo ndi mʼbado uwu ndi kuwutsutsa pakuti iwo analapa Yona atalalikira ndipo tsopano wamkulu kuposa Yona ali pano.
Nanawe asay pirda galas hayssa ha yeletara dendidi ha yeleta bolla pirdana; gasoykka Nanawe asay Yoonaasa markatethan maroteth gelida gishasa. Hekko Yoonaasappe adhizadey han dees.
42 Mfumu yayikazi yakummwera idzayimirira pa tsiku lachiweruzo ndi mʼbado uwu ndipo idzawutsutsa pakuti inachokera kumathero a dziko lapansi kudzamva nzeru za Solomoni, ndipo pano pali woposa Solomoni.
Dugge baga dere kawoya Solomoone erateth siyanas bitta gaxappe dendada yidda gish pirda galas iza hayssa yeletethara dendada ha yeletetha bolla pirdana. Hekko Solomooneppe adhizadey hayssan dess.
43 “Pamene mzimu woyipa utuluka mwa munthu, umadutsa malo wopanda madzi kufunafuna malo opumulira ndipo suwapeza.
Tuna ayanay asappe kezidi sheemppo demanas hathi baynda mela bitan dabures, gido attin ba koyiza shemppo demena.
44 Pamenepo umati, ‘Ndidzabwerera ku nyumba yanga komwe ndinatuluka.’ Pamene ufika, upeza mopanda kanthu, mosesedwa ndi mokonzedwa bwino.
Hessappe qasse kasse ta dizaso siimma bana gidi beniso izi simishin kasse izi dizasoy aykoyne baynda mela keth gididi geyidine gigeti dizaysa deemess.
45 Kenaka umapita kukatenga mizimu ina isanu ndi iwiri yoyipa kwambiri kuposa uwowo ndipo imapita ndi kukakhala mʼmenemo. Choncho khalidwe lotsiriza la munthu uyu limakhala loyipa kwambiri kuposa loyambalo. Umo ndi mmene zidzakhalire ndi mʼbado oyipawu.”
Hessafe bidi hara beppe itiza lapun iitta ayanata benara ekidi yeess. Istika he uran gelidi deyana. He uras kasse dusafe guye dusay iita gidana. Haysa iitta yeletethaskka hessa mala hanana.
46 Pamene Yesu anali kuyankhulabe ndi gulu la anthu, amayi ndi abale ake anayimirira kunja, akufuna kuyankhulana naye.
Yesusay asas yotishin iza ayiyane ishati iza yochana koyidi karen eeqidashe;
47 Wina anamuwuza Iye kuti, “Amayi ndi abale anu ayima kunjaku akufuna kuyankhulana nanu.”
Issi uray hekko ne ayane ne ishati nena hasa7isanas karen eeqidi nena koyetes gidess.
48 Iye anayankha kuti, “Amayi anga ndani ndipo abale anga ndi ndani?”
Yesusaykka ta aya oone? ta ishatich isti oonante? gidess.
49 Ndipo akuloza ophunzira ake, Iye anati, “Awa ndiwo amayi anga ndi abale anga.
Be kushera bena kalizaytakko malatidi, ta ayane ta ishati haytanta.
50 Pakuti aliyense amene achita chifuniro cha Atate anga akumwamba ndiye mʼbale wanga, mlongo wanga ndi amayi anga.”
Salon diza ta aawa shene othizayti wurikka tass isha michchonne ayo gidess.

< Mateyu 12 >