< Mateyu 11 >

1 Ndipo Yesu atamaliza kulangiza ophunzira ake khumi ndi awiri aja, anachoka kumeneko kupita kukaphunzitsa ndi kukalalikira ku mizinda ya ku Galileya.
ittha. m yii"su. h svadvaada"sa"si. syaa. naamaaj naapana. m samaapya pure pura upade. s.tu. m susa. mvaada. m pracaarayitu. m tatsthaanaat pratasthe|
2 Yohane ali mʼndende anamva zimene Khristu ankachita, ndipo anatumiza ophunzira ake kukamufunsa Iye.
anantara. m yohan kaaraayaa. m ti. s.than khri. s.tasya karmma. naa. m vaartta. m praapya yasyaagamanavaarttaasiit saeva ki. m tva. m? vaa vayamanyam apek. si. syaamahe?
3 Anamufunsa kuti, “Kodi Inu ndinu uja ankanena kuti mudzabwerayu kapena tidikire wina?”
etat pra. s.tu. m nijau dvau "si. syau praahi. not|
4 Yesu anayankha kuti, “Bwererani ndi kukamuwuza Yohane zimene mwamva ndi kuona.
yii"su. h pratyavocat, andhaa netraa. ni labhante, kha ncaa gacchanti, ku. s.thina. h svasthaa bhavanti, badhiraa. h "s. r.nvanti, m. rtaa jiivanta utti. s.thanti, daridraa. naa. m samiipe susa. mvaada. h pracaaryyata,
5 Osaona akuona, olumala akuyenda, akhate akuchiritsidwa, osamva akumva, akufa akuukitsidwa ndipo Uthenga Wabwino ukulalikidwa kwa osauka.
etaani yadyad yuvaa. m "s. r.nutha. h pa"syatha"sca gatvaa tadvaarttaa. m yohana. m gadata. m|
6 Odala ndi munthu amene sakhumudwa chifukwa cha Ine.”
yasyaaha. m na vighniibhavaami, saeva dhanya. h|
7 Pamene ophunzira a Yohane ankachoka, Yesu anayamba kuyankhula kwa gulu la anthu za Yohane kuti, “Kodi munkapita ku chipululu kuti mukaone chiyani? Kodi bango logwedezeka ndi mphepo?
anantara. m tayo. h prasthitayo ryii"su ryohanam uddi"sya janaan jagaada, yuuya. m ki. m dra. s.tu. m vahirmadhyepraantaram agacchata? ki. m vaatena kampita. m nala. m?
8 Nanga munkapita kukaona chiyani, munthu wovala zokongola? Ayi, wovala zokongola amakhala mʼnyumba za mafumu.
vaa ki. m viik. situ. m vahirgatavanta. h? ki. m parihitasuuk. smavasana. m manujameka. m? pa"syata, ye suuk. smavasanaani paridadhati, te raajadhaanyaa. m ti. s.thanti|
9 Nanga munkapita kukaona chiyani? Mneneri kodi? Inde ndikuwuzani kuti munkakaona woposa mneneri.
tarhi yuuya. m ki. m dra. s.tu. m bahiragamata, kimeka. m bhavi. syadvaadina. m? tadeva satya. m| yu. smaanaha. m vadaami, sa bhavi. syadvaadinopi mahaan;
10 Uyu ndi amene malemba akunena za iye kuti, “Ine ndidzatuma mthenga wanga patsogolo panu amene adzakonza njira yanu.
yata. h, pa"sya svakiiyaduutoya. m tvadagre pre. syate mayaa| sa gatvaa tava panthaana. m smayak pari. skari. syati|| etadvacana. m yamadhi likhitamaaste so. aya. m yohan|
11 Zoonadi, Ine ndikuwuzani kuti pakati pa obadwa ndi mkazi sipanaoneke wina aliyense wamkulu woposa Yohane Mʼbatizi; komatu amene ndi wamngʼono kwambiri mu ufumu wakumwamba ndi wamkulu koposa iye.
apara. m yu. smaanaha. m tathya. m braviimi, majjayitu ryohana. h "sre. s.tha. h kopi naariito naajaayata; tathaapi svargaraajyamadhye sarvvebhyo ya. h k. sudra. h sa yohana. h "sre. s.tha. h|
12 Kuyambira masiku a Yohane Mʼbatizi mpaka tsopano, ufumu wakumwamba ndi wolimbirana ndipo anthu amphamvu okha ndi amene akuwulanda.
apara nca aa yohano. adya yaavat svargaraajya. m balaadaakraanta. m bhavati aakramina"sca janaa balena tadadhikurvvanti|
13 Pakuti aneneri onse ndi malamulo ananenera kufikira nthawi ya Yohane.
yato yohana. m yaavat sarvvabhavi. syadvaadibhi rvyavasthayaa ca upade"sa. h praakaa"syata|
14 Ndipo ngati inu mufuna kulandira izi, iyeyu ndi Eliya amene ankanena kuti adzabwera uja.
yadi yuuyamida. m vaakya. m grahiitu. m "saknutha, tarhi "sreya. h, yasyaagamanasya vacanamaaste so. ayam eliya. h|
15 Iye amene ali ndi makutu amve.
yasya "srotu. m kar. nau sta. h sa "s. r.notu|
16 “Kodi mʼbado uwu ndingawufanizire ndi chiyani? Uli ngati ana opezeka mʼmisika amene akuyitana anzawo nʼkumati:
ete vidyamaanajanaa. h kai rmayopamiiyante? ye baalakaa ha. t.ta upavi"sya sva. m sva. m bandhumaahuuya vadanti,
17 “‘Tinakuyimbirani zitoliro, koma inu simunavine; ife tinayimba nyimbo zamaliro, koma inu simunalire.’
vaya. m yu. smaaka. m samiipe va. m"siiravaadayaama, kintu yuuya. m naan. rtyata; yu. smaaka. m samiipe ca vayamarodima, kintu yuuya. m na vyalapata, taad. r"sai rbaalakaista upamaayi. syante|
18 Pakuti Yohane sanabwerere kudya kapena kumwa koma iwo ankanena kuti, ‘Iye anali ndi chiwanda.’
yato yohan aagatya na bhuktavaan na piitavaa. m"sca, tena lokaa vadanti, sa bhuutagrasta iti|
19 Mwana wa Munthu anabwera ndi kumadya ndi kumwa koma iwo akuti, ‘Munthu wadyera, woledzera, bwenzi la amisonkho ndi bwenzi la ochimwa.’ Koma nzeru imatsimikizika kuti ndi yolondola mwa ntchito zake.”
manujasuta aagatya bhuktavaan piitavaa. m"sca, tena lokaa vadanti, pa"syata e. sa bhoktaa madyapaataa ca. n.daalapaapinaa. m bandha"sca, kintu j naanino j naanavyavahaara. m nirdo. sa. m jaananti|
20 Pamenepo Yesu anayamba kudzudzula mizinda imene zodabwitsa zake zambiri zinachitikamo, chifukwa chakuti sinatembenuke mtima.
sa yatra yatra pure bahvaa"scaryya. m karmma k. rtavaan, tannivaasinaa. m mana. hparaav. rttyabhaavaat taani nagaraa. ni prati hantetyuktaa kathitavaan,
21 “Tsoka kwa iwe Korazini! Tsoka kwa iwe Betisaida! Ngati zodabwitsa zimene zinachitika mwa iwe zikanachitidwa mu Turo ndi Sidoni, iwo akanalapa kale atavala ziguduli ndi kudzola phulusa.
haa koraasiin, haa baitsaide, yu. smanmadhye yadyadaa"scaryya. m karmma k. rta. m yadi tat sorasiidonnagara akaari. syata, tarhi puurvvameva tannivaasina. h "saa. navasane bhasmani copavi"santo manaa. msi paraavartti. syanta|
22 Koma ndikuwuzani inu kuti pa tsiku lachiweruzo mlandu wa Turo ndi Sidoni udzachepako kusiyana ndi wanu.
tasmaadaha. m yu. smaan vadaami, vicaaradine yu. smaaka. m da"saata. h sorasiidono rda"saa sahyataraa bhavi. syati|
23 Ndipo iwe Kaperenawo, kodi udzakwezedwa kufika kumwamba? Ayi, udzatsitsidwa mpaka pansi kufika ku Hade. Ngati zodabwitsa zimene zinachitika mwa iwe, zikanachitika mu Sodomu, bwenzi iye alipo kufikira lero. (Hadēs g86)
apara nca bata kapharnaahuum, tva. m svarga. m yaavadunnatosi, kintu narake nik. sepsyase, yasmaat tvayi yaanyaa"scaryyaa. ni karmma. nyakaari. sata, yadi taani sidomnagara akaari. syanta, tarhi tadadya yaavadasthaasyat| (Hadēs g86)
24 Koma Ine ndikuwuzani kuti pa tsiku la chiweruziro mlandu wa Sodomu udzachepako kusiyana ndi wanu.”
kintvaha. m yu. smaan vadaami, vicaaradine tava da. n.data. h sidomo da. n.do sahyataro bhavi. syati|
25 Pa nthawi imeneyo Yesu anati, “Ine ndikukuyamikani Inu Atate Ambuye akumwamba ndi dziko lapansi, chifukwa Inu mwawabisira zinthu izi anzeru ndi ophunzira ndi kuziwulula kwa ana angʼonoangʼono.
etasminneva samaye yii"su. h punaruvaaca, he svargap. rthivyorekaadhipate pitastva. m j naanavato vidu. sa"sca lokaan pratyetaani na prakaa"sya baalakaan prati prakaa"sitavaan, iti hetostvaa. m dhanya. m vadaami|
26 Inde, Atate, ichi chinali chokukomerani Inu.
he pita. h, ittha. m bhavet yata ida. m tvad. r.s. taavuttama. m|
27 “Zinthu zonse zapatsidwa kwa Ine ndi Atate anga. Palibe mmodzi amene adziwa Mwana kupatula Atate ndipo palibe mmodzi amene adziwa Atate kupatula Mwana ndi kwa iwo amene Mwana awasankha kuwawululira.
pitraa mayi sarvvaa. ni samarpitaani, pitara. m vinaa kopi putra. m na jaanaati, yaan prati putre. na pitaa prakaa"syate taan vinaa putraad anya. h kopi pitara. m na jaanaati|
28 “Idzani kwa Ine, inu nonse otopa ndi olemedwa ndipo Ine ndidzakupatsani mpumulo.
he pari"sraantaa bhaaraakraantaa"sca lokaa yuuya. m matsannidhim aagacchata, aha. m yu. smaan vi"sramayi. syaami|
29 Senzani goli langa ndipo phunzirani kwa Ine, pakuti ndine wofatsa ndi wodzichepetsa. Ndipo inu mudzapeza mpumulo wa miyoyo yanu.
aha. m k. sama. na"siilo namramanaa"sca, tasmaat mama yuga. m sve. saamupari dhaarayata matta. h "sik. sadhva nca, tena yuuya. m sve sve manasi vi"sraama. m lapsyadhbe|
30 Pakuti goli langa ndi losavuta ndipo katundu wanga ndi wopepuka.”
yato mama yugam anaayaasa. m mama bhaara"sca laghu. h|

< Mateyu 11 >