< Mateyu 1 >

1 Buku lofotokoza za mʼbado wa Yesu Khristu mwana wa Davide, mwana wa Abrahamu:
Kitabu ka ukoo wang'wa Yesu Kilisto ng'wana wang'wa Daudi, ng'wana wang'wa Ibrahimu.
2 Abrahamu anabereka Isake, Isake anabereka Yakobo, Yakobo anabereka Yuda ndi abale ake.
Ibrahimu ae tata wang'wa Isaka, nu Isaka tata wang'wa Yakobo, nu Yakobo tata wang'wa Yuda nialuna akwe.
3 Yuda anabereka Perezi ndi Zara, amene amayi awo anali Tamara. Perezi anabereka Hezironi, Hezironi anabereka Aramu.
U Yuda ae tata wang'wa Peresi nu Sera kung'wa Tamari, Peresi tata wang'wa Hezeroni, nu Hezeroni tata wang'wa Ramu.
4 Aramu anabereka Aminadabu, Aminadabu anabereka Naasoni, Naasoni anabereka Salimoni.
U Ramu ae tata wang'wa Aminadabu, Aminadabu tata wang'wa Nashoni, nu Nashoni tata wang'wa Salimoni.
5 Salimoni anabereka Bowazi amene amayi ake anali Rahabe, Bowazi anabereka Obedi amene amayi ake anali Rute, Obedi anabereka Yese.
Salimoni ae tata wang'wa Boazi kung'wa Rahabu, u Boazi tata wang'wa Obedi kung'wa Ruthi, u Obedi tata wang'wa Yese,
6 Yese anabereka Mfumu Davide. Ndipo Davide anabereka Solomoni, amene amayi ake anali mkazi wa Uriya.
u Yese ae tata wang'wa mtemi Daudi, u Daudi ae tata wang'wa Sulemani kumu sungu wang'wa Uria.
7 Solomoni anabereka Rehabiamu, Rehabiamu anabereka Abiya, Abiya anabereka Asa,
Sulemani ae tata wang'wa Rehoboamu, Rehoboamu tata wang'wa Abiya, Abiya tata wang'wa Asa.
8 Asa anabereka Yehosafati, Yehosafati anabereka Yoramu, Yoramu anabereka Uziya.
Asa ae tata wang'wa Yehoshafati, Yehoshafati tata wang'wa Yoramu, nu Yoramu tata wang'wa Uzia.
9 Uziya anabereka Yotamu, Yotamu anabereka Ahazi, Ahazi anabereka Hezekiya.
Uzia ae tata wang'wa Yothamu, u Yothamu ae tata wang'wa Ahazi, u Ahazi tata wang'wa Hezekia.
10 Hezekiya anabereka Manase, Manase anabereka Amoni, Amoni anabereka Yosiya.
Hezekia ae tata wang'wa Manase, u Manase tata wang'wa Amoni nu Amoni tata wang'wa Yosia.
11 Yosiya anali atabala Yekoniya ndi abale ake pamene Ayuda anatengedwa ukapolo kupita ku Babuloni.
U Yosia ae tata wang'wa Yekonia nialuna akwe naiahoilwe kulongola ku Babeli.
12 Ali ku ukapolo ku Babuloni, Yekoniya anabereka Salatieli, Salatieli anabereka Zerubabeli.
Nai aholwa kulongola ku Babeli, Yekonia ae tata wang'wa Shetieli, u Shetieli ai sekulu wakwe nu Zerubabeli.
13 Zerubabeli anabereka Abiudi, Abiudi anabereka Eliakimu, Eliakimu anabereka Azoro.
Zerubabeli ai tata wang'wa Abiudi, Abiudi tata wang'wa Eliakimu, nu Eliakimu tata wang'wa Azori.
14 Azoro anabereka Zadoki, Zadoki anabereka Akimu, Akimu anabereka Eliudi.
Azori ai tata wang'wa Zadoki, nu Zadoki tata wang'wa Akimu, nu Akimu tata wang'wa Eliudi.
15 Eliudi anabereka Eliezara, Eliezara anabereka Matani, Matani anabereka Yakobo.
Eliudi ae tata wang'wa Elieza, Elieza tata wang'wa Matani nu Matani tata wang'wa Yakobo.
16 Yakobo anabereka Yosefe, mwamuna wa Mariya. Mariyayu ndiye anabereka Yesu wotchedwa Khristu.
U Yakobo ai tata wang'wa Yusufu mugoha wang'wa Mariamu, kukeela ng'wenso u Yesu akatugwa, naewitangilwe Kilisto.
17 Kuyambira pa Abrahamu mpaka pa Davide, pali mibado khumi ndi inayi. Ndipo kuyambira pa Davide mpaka pamene Ayuda anatengedwa kupita ku ukapolo ku Babuloni, pali mibado khumi ndi inayi. Ndiponso kuyambira nthawi ya ukapolo ku Babuloni mpaka pamene Khristu anabadwa, palinso mibado khumi ndi inayi.
Wileli wehi puma u Ibrahimu nu Daudi ae wileli wikumi na inne, kupuma u Daudi nukunolwa kulongola ku Babeli ae wileli wi kumi na inne, nu kumakuholwa kulongola ku Babeli kupika kung'wa Yesu ae wileli ikumi na inne.
18 Kubadwa kwa Yesu Khristu kunali motere: Amayi ake, Mariya, anapalidwa ubwenzi ndi Yosefe, koma asanagone malo amodzi, anapezeka ali woyembekezera mwana mwa mphamvu ya Mzimu Woyera.
Kutugwa kung'wa Yesu Kilisto aeitwile ite, Mariamu, auligigwe nu Yusufu, akaze akile kutankanya, akigeeleka ukete nda ang'wau ng'welu.
19 Popeza Yosefe mwamuna wake anali munthu wolungama, sanafune kumuchititsa manyazi pomuleka poyera. Choncho anaganiza zomuleka mosaonetsera.
Umugoha wakwe u Yusufu, ae muntu wa tai, singa akalowa kumuhumya uminyala u Mariamu. Akahia amuleke kenkunku.
20 Koma akuganiza zimenezi, taonani, mngelo wa Ambuye anamuonekera mʼmaloto nati, “Yosefe mwana wa Davide, usaope kumutenga Mariya kukhala mkazi wako, chifukwa mwana akuyembekezerayo ndi wochokera kwa Mzimu Woyera.
Naukusiga ulukani nulanso, umalaika wang'wa Itunda akamizeela kukeela ndoti. Akalunga, “Yusufu ng'wana wang'wa Daudi, leka kugopa kumuhola u Mariamu anga msungu wako, nsoko inda nutite upatile kungulu ya ng'waung'welu.
21 Ndipo adzabala mwana wamwamuna, udzamutcha dzina lake Yesu; pakuti Iyeyo adzapulumutsa anthu ake ku machimo awo.”
Ukitunguila ng'wana mgoha ni lina lakwe ukumitanga Yesu, kunsoko ukuaguna antu ni milandu ao.
22 Zonsezi zinachitika kukwaniritsa zimene Ambuye ananena mwa mneneri kuti,
Aya ihi aigelekile kukondanilya iko naikiligitigwe ni Tunda kukeela anyakidagu, akalunga.
23 “Onani namwali adzakhala woyembekezera ndipo adzabala mwana wamwamuna, ndipo mwanayo adzamutcha Imanueli,” kutanthauza kuti, “Mulungu ali nafe.”
Gozi umunanso ukuhola nda nukitunguela ng'wana mugoha, ilina lakwe ukitangwa Immanueli, nsoko akwe “Itunda palung'wi nu sese.”
24 Yosefe atadzuka, anachita zomwe mngelo wa Ambuye uja anamulamulira. Iye anamutenga Mariya kukhala mkazi wake.
Yusufu akauka kupuma mutulo akituma anga naulagiigwe nu malaika akamuhola akatula msungu wakwe.
25 Koma sanagone malo amodzi mpaka mwanayo atabadwa ndipo anamutcha dzina lake Yesu.
Palung'wi nayo nanso singa aeihugee, singa akatugwa ung'wana akamitanga lina lakwe Yesu.

< Mateyu 1 >