< Marko 4 >

1 Nthawi inanso Yesu atakhala mʼmbali mwa nyanja, anayamba kuphunzitsa. Gulu lalikulu la anthu linasonkhana momuzungulira kotero kuti Iye analowa mʼbwato lomwe linali pa nyanja nakhalamo, anthu onse ali pa mtunda mʼmbali mwa madzi.
Jednou Ježíš opět učil na břehu jezera. A protože se kolem něho znovu shromáždily davy lidí, nastoupil do člunu a odtud mluvil k těm, kteří byli na břehu.
2 Anawaphunzitsa zinthu zambiri mʼmafanizo, ndipo mʼchiphunzitso chake anati:
Ježíš své učení často vkládal do zvláštních obrazů – podobenství. Toto je jedno z nich:
3 “Tamverani! Mlimi anapita kukafesa mbewu zake.
„Poslouchejte! Jeden rolník se vydal na pole, aby zasel obilí.
4 Akufesa, mbewu zina zinagwera mʼmbali mwa njira, ndipo mbalame zinabwera ndi kuzidya.
Ne každé zrno však padlo na vhodnou půdu. Některá se dostala na okraj cesty, kde je sezobali ptáci.
5 Zina zinagwa pa malo a miyala pamene panalibe dothi lambiri. Zinamera mofulumira chifukwa panalibe dothi lambiri.
Jiná padla na skálu, kde bylo jen málo půdy.
6 Koma dzuwa litakwera, mbewuzo zinapserera, ndipo zinawuma chifukwa zinalibe mizu.
Tam sice zrna brzy vyklíčila, ale ve slunečním žáru osení uschlo, protože kořínky v mělké vrstvě země neměly dost vláhy.
7 Mbewu zina zinagwa pa minga, ndipo mingayo inayanga ndi kuzirepheretsa kukula.
Jiná zrna zapadla mezi bodláčí, které záhy mladé rostlinky udusilo, takže ani nenasadily klasy.
8 Mbewu zinanso zinagwa pa nthaka yabwino ndipo zinamera, zinakula ndi kubereka zipatso, zina zochuluka makumi atatu, zina makumi asanu ndi limodzi ndi zina 100.”
Ovšem to zrní, které padlo do úrodné půdy, přineslo třicetinásobný, jiné dokonce šedesáti – až stonásobný užitek.“
9 Pamenepo Yesu anati, “Amene ali ndi makutu akumva, amve.”
„Kdo má uši k naslouchání, ten ať poslouchá a přemýšlí, “uzavřel Ježíš.
10 Ali yekha, ophunzira ndi ena omuzungulira, anamufunsa za mafanizo.
Později, když byl sám se svými dvanácti učedníky, ptali se ho: „Jak máme tvým podobenstvím rozumět?“
11 Iye anawawuza kuti, “Chinsinsi cha ufumu wa Mulungu chapatsidwa kwa inu. Koma kwa amene ali kunja zinthu zonse zinenedwa mʼmafanizo:
„Vy, kteří mi býváte nablízku, “odpověděl, „jste už pochopili mnohé z tajemství Božího království. Ale těm, co jsou ještě opodál, se to snažím vysvětlovat v podobenstvích.
12 kotero kuti, “‘Kupenya mudzapenya koma osaona kanthu, kumva mudzamva koma osamvetsetsa, kuti mwina angatembenuke ndi kukhululukidwa!’”
Je však o nich psáno v proroctví: Dívají se, a nevidí, poslouchají, a přece nerozumějí, a tak nejsou ochotni obrátit se k Bohu, aby jim odpustil jejich viny.
13 Pamenepo Yesu anawawuza kuti, “Kodi simukulimvetsa fanizoli? Kodi nanga mudzazindikira bwanji fanizo lina lililonse?
Jestliže ovšem ani vy nechápete tento jednoduchý obraz, jak potom porozumíte všem dalším, které vám chci vyprávět?
14 Wofesa amafesa mawu.
Zde je tedy výklad: Tím rolníkem, o kterém jsem mluvil, je každý, kdo lidem přináší Boží poselství, aby je zasel do jejich života jako dobrou setbu.
15 Anthu ena ali ngati mbewu za mʼmbali mwa njira, mʼmene mawu amafesedwamo. Akangowamva, Satana amabwera ndi kuchotsa mawu amene anafesedwa mwa iwo.
Srdce některých posluchačů je tvrdé jako ušlapaná cesta. Satan okamžitě přichází a usiluje o to, aby zapomněli, co slyšeli.
16 Ena, monga mbewu zofesedwa pa miyala, amamva mawu ndipo nthawi yomweyo amawalandira ndi chimwemwe.
Mělká skalnatá půda představuje srdce nestálých lidí. Boží poselství vyslechnou a radostně přijmou,
17 Koma popeza alibe mizu, amakhala kwa kanthawi kochepa. Mavuto kapena masautso akafika chifukwa cha mawu, amagwa mofulumira.
jsou však povrchní a slovo u nich nepronikne do hloubky. I když si zpočátku vedou dobře, odpadají, jakmile mají pro víru trpět.
18 Komabe ena, monga mbewu zofesedwa pakati pa minga, amamva mawu;
Půda zaplevelená bodláčím je obrazem lidí, kteří dobrou Boží zprávu sice vyslechnou a přijmou,
19 koma nkhawa zamoyo uno, chinyengo cha chuma ndi zokhumba za zinthu zina zimabwera ndi kutchinga mawu, ndipo amawachititsa kukhala osabala chipatso. (aiōn g165)
ale všední starosti, záliba v majetku a touha po blahobytu Boží poselství v srdci udusí, takže zůstane bez užitku. (aiōn g165)
20 Ena, ngati mbewu zofesedwa pa nthaka yabwino, amamva mawu, nawalandira, ndi kubereka zipatso zokwanira makumi atatu, makumi asanu ndi limodzi, kapena ngakhale 100 kuwonjezera pa zomwe zinafesedwa.”
Úrodné půdě se podobají ti, kteří bez výhrad přijímají Boží zvěst, a proto mohou přinést bohatou sklizeň – někteří dokonce mimořádnou sklizeň.“
21 Iye anawawuza kuti, “Kodi umatenga nyale ndi kuyiika pansi pa mbiya kapena pansi pa bedi? Mʼmalo mwake, kodi simuyika pa choyikapo chake?
„Když někdo z vás rozsvítí lampu, zakryje ji snad nádobou nebo ji strčí pod postel, aby zakryl její světlo? Určitě ne! Umístí ji tak, aby svítila.
22 Pakuti chilichonse chobisika chidzayenera kuwululika, ndi chilichonse chachinsinsi chidzayenera kuonekera poyera.
Všechno, co je dosud skryto, vyjde najevo a tomu, co je nesrozumitelné, bude porozuměno. Dobře poslouchejte, co vám říkám. Kolik jste ochotni přijmout, tolik dostanete a ještě vám bude přidáno.
23 Ngati wina ali ndi makutu akumva, amve.”
24 Anapitiriza nati, “Ganizirani mosamala zimene mukumva, ndi muyeso umene mugwiritsa ntchito, mudzayesedwa nawo, ndipo ngakhale kwambiri.
25 Amene ali nazo adzapatsidwa zochuluka; amene alibe, ngakhale zimene ali nazo zidzachotsedwa kwa iwo.”
Kdo už něco pochopil, porozumí ještě víc; kdo o to nestojí, přijde o všechno.“
26 Iye anatinso, “Umu ndi mmene ulili ufumu wa Mulungu. Munthu amafesa mbewu mʼnthaka.
Dále Ježíš vyprávěl jiné podobenství: „S Božím královstvím je to jako s rolníkem, který oseje pole a odejde.
27 Usiku ndi usana, kaya agona kapena adzuka, mbewu imamera ndi kukula, ngakhale sadziwa mmene zimachitikira.
Dny plynou, zrno vyklíčí a roste ve dne v noci, aniž by se o ně musel nějak starat nebo mu pomáhat.
28 Nthaka pa yokha imatulutsa mbewu, umayamba mʼmera, kenaka ngala, kenaka mbewu yokhwima mʼngalayo.
Půda sama dává semenu, co potřebuje k růstu. Nejdříve vzejde klíček, pak vyroste stéblo, potom klas.
29 Mbewuyo ikangokhwima, amayimweta chifukwa nthawi yokolola yakwana.”
A když v něm nakonec dozraje zrno, přijde rolník a sklidí je.“
30 Ndipo anatinso, “Kodi tinene kuti ufumu wa Mulungu ufanana ndi chiyani, kapena ndi fanizo lotani limene tidzagwiritsa ntchito pakuwufotokozera?
„Jak ještě znázornit Boží království? K čemu ho přirovnat?“uvažoval Ježíš.
31 Uli ngati mbewu ya mpiru imene ndi mbewu yayingʼono kwambiri yomwe mumadzala mʼnthaka.
„Je to s ním jako se seménkem hořčice.
32 Koma ikadzalidwa, imakula ndi kukhala yayikulu koposa mbewu zina zonse za mʼmunda ndipo mʼnthambi zake zazikulu mbalame zamlengalenga zimadzapuma pa mthunzi wake.”
To sice patří mezi nejmenší semena, ale vyroste z něho největší bylina na poli. Na jejích větvích mohou dokonce hnízdit ptáci.“
33 Ndi mafanizo ambiri onga awa Yesu anayankhula mawu kwa iwo, monga mmene akanatha kumvetsa.
Ještě mnoho podobných obrazů Ježíš použil, aby lidem přiblížil svoje učení.
34 Iye sananene kanthu kwa iwo osagwiritsa ntchito fanizo. Koma ali yekha ndi ophunzira ake, ankawatanthauzira zonse.
Když mluvil veřejně, používal výhradně přirovnání. Když však potom býval se svými učedníky o samotě, všechno jim vysvětloval.
35 Tsiku limenelo atafika madzulo, anawuza ophunzira ake kuti, “Tiyeni tiwolokere tsidya lina.”
K večeru toho dne vyzval Ježíš své učedníky: „Přeplavme se na druhou stranu jezera.“
36 Atasiya gulu la anthu mʼmbuyo, anamutenga Iye, napita naye monga momwe anali mʼbwatolo. Panalinso mabwato ena pamodzi ndi Iye.
Odrazili tedy s lodí, ve které seděl, a vzdalovali se od zástupů na břehu. Několik člunů však vyplulo za nimi.
37 Mphepo yamkuntho inabuka, ndipo mafunde anawomba bwatolo, kotero kuti linali pafupi kumira.
Zanedlouho se strhla silná větrná bouře. Vysoké vlny dorážely na člun a ten se začal plnit vodou.
38 Pa nthawi imeneyi Yesu anali akugona atatsamira pilo kumbuyo kwa bwato. Ophunzira anamudzutsa nati kwa Iye, “Aphunzitsi, kodi simukusamala kuti timira?”
Ježíš však klidně spal na zádi, s poduškou pod hlavou. Učedníci ho probudili: „Mistře, tobě je jedno, že se potápíme?“
39 Yesu anauka nadzudzula mphepo nati kwa mafunde, “Chete! Khala bata!” Pamenepo mphepo inaleka ndipo kunachita bata.
Ježíš vstal, okřikl vítr a poručil vlnám: „Uklidněte se!“V tu chvíli se vítr utišil a kolem se rozhostil klid.
40 Iye anati kwa ophunzira ake, “Muli ndi mantha chifukwa chiyani? Kodi mukanalibe chikhulupiriro?”
Pak se Ježíš obrátil na učedníky: „Proč jste se tolik báli? Copak mi nedůvěřujete?“
41 Iwo anachita mantha nafunsana wina ndi mnzake kuti, “Uyu ndani? Ngakhale mphepo ndi nyanja zimumvera Iye!”
Byli tím vším ohromeni a ptali se jeden druhého: „Kdo to jen může být, že ho poslouchá vítr i voda?“

< Marko 4 >