< Marko 3 >

1 Nthawi inanso analowa mʼsunagoge, ndipo munthu wa dzanja lolumala anali momwemo.
I uðe opet u zbornicu, i ondje bješe èovjek sa suhom rukom.
2 Ena a iwo anafunafuna chifukwa chakuti akamuneneze Yesu, potero anamuyangʼanitsitsa kuti aone ngati angamuchiritse tsiku la Sabata.
I motrahu za njim neæe li ga u subotu iscijeliti da ga okrive.
3 Yesu anati kwa munthu wolumala dzanjayo, “Imirira, bwera kuno kutsogolo.”
I reèe èovjeku sa suhom rukom: stani na srijedu.
4 Ndipo Yesu anawafunsa kuti, “Kodi chololedwa ndi chiyani pa tsiku la Sabata: kuchita chabwino kapena kuchita choyipa, kupulumutsa moyo kapena kupha?” Koma iwo anakhala chete.
I reèe im: valja li u subotu dobro èiniti ili zlo èiniti? dušu održati, ili pogubiti? A oni muèahu.
5 Yesu anawayangʼana ndi mkwiyo ndipo powawidwa mtima chifukwa cha mitima yawo yowuma anati kwa munthuyo, “Wongola dzanja lako.” Iye analiwongola, ndipo dzanja lake linachira.
I pogledavši na njih s gnjevom od žalosti što su im onako srca odrvenila reèe èovjeku: pruži ruku svoju. I pruži; i posta ruka zdrava kao i druga.
6 Kenaka Afarisi anatuluka nayamba kukonza chiwembu ndi Aherode mmene angamuphere Yesu.
I izišavši fariseji odmah uèiniše za njega vijeæu s Irodovcima kako bi ga pogubili.
7 Yesu anachoka pamodzi ndi ophunzira ake napita ku nyanja, ndipo gulu lalikulu la anthu lochokera ku Galileya linamutsata.
A Isus otide s uèenicima svojijem k moru; i mnogi narod iz Galileje ide za njim i iz Judeje;
8 Atamva zonse zimene amachita, anthu ambiri anabwera kwa Iye kuchokera ku Yudeya, Yerusalemu, Idumeya ndi madera a ku tsidya kwa mtsinje wa Yorodani ndi ozungulira Turo ndi Sidoni.
I iz Jerusalima i iz Idumeje i ispreko Jordana i od Tira i Sidona mnoštvo veliko èuvši šta on èini doðe k njemu.
9 Chifukwa cha gulu la anthu, anawuza ophunzira ake kuti apezeretu bwato likhale, kuti anthu angamupanikize.
I reèe uèenicima svojijem da bude laða u njega gotova zbog naroda, da mu ne dosaðuje.
10 Pakuti anachiritsa ambiri, kotero kuti iwo amene anali ndi matenda amakankhana kutsogolo kuti amukhudze.
Jer mnoge iscijeli tako da navaljivahu na njega koji bijahu nakaženi bolestima da ga se dotaknu.
11 Nthawi iliyonse mizimu yoyipa ikamuona, imagwa pansi pamaso pake ndi kufuwula kuti, “Inu ndinu Mwana wa Mulungu!”
I dusi neèisti kad ga viðahu, pripadahu k njemu i vikahu govoreæi: ti si sin Božij.
12 Koma anayichenjeza mwamphamvu kuti isanene kuti Iye anali ndani.
I mnogo im prijeæaše da ga ne prokažu.
13 Yesu anakwera ku phiri ndipo anayitana amene anawafuna, ndipo anabwera kwa Iye.
I iziðoše na goru, i dozva koje on šæaše; i doðoše mu.
14 Iye anasankha khumi ndi awiri, nawayika akhale atumwi; pokhala ndi Iye aziwatuma kukalalikira
I postavi dvanaestoricu da budu s njim, i da ih pošilje da propovijedaju,
15 ndi kuti akhale ndi ulamuliro wotulutsa ziwanda.
I da imaju vlast da iscjeljuju od bolesti, i da izgone ðavole:
16 Awa ndi khumi ndi awiri amene anawasankha: Simoni (amene anapatsidwa dzina lakuti Petro);
Prvoga Simona, i nadjede mu ime Petar;
17 Yakobo mwana wa Zebedayo, ndi mʼbale wake Yohane (iwowa anawapatsa dzina lakuti Bowanege, ndiye kuti ana a bingu);
I Jakova Zevedejeva i Jovana brata Jakovljeva, i nadjede im imena Voanerges, koje znaèi sinovi gromovi;
18 Andreya, Filipo, Bartumeyu, Mateyu, Tomasi, Yakobo mwana wa Alufeyo, Tadeyo, Simoni Zelote,
I Andriju i Filipa i Vartolomija i Mateja i Tomu i Jakova Alfejeva i Tadiju i Simona Kananita,
19 ndi Yudasi Isikarioti, amene anamupereka Iye.
I Judu Iskariotskoga, koji ga i izdade.
20 Pambuyo pake Yesu analowa mʼnyumba, ndipo gulu la anthu linasonkhananso, kotero kuti Iye pamodzi ndi ophunzira ake sanapeze mpata kuti adye.
I doðoše u kuæu, i sabra se opet narod da ne mogahu ni hljeba jesti.
21 Anthu a ku banja lake atamva zimenezi, anapita kuti akamutenga, pakuti ankanena kuti, “Wazungulira mutu.”
I èuvši to rod njegov iziðoše da ga uhvate; jer govorahu da je izvan sebe.
22 Ndipo aphunzitsi amalamulo omwe anachokera ku Yerusalemu anati, “Iye wagwidwa ndi Belezebabu! Ndi ulamuliro wa mkulu wa ziwanda akutulutsa ziwanda.”
A književnici koji bijahu sišli iz Jerusalima govorahu: u njemu je Veelzevul; i: on pomoæu kneza ðavolskoga izgoni ðavole.
23 Pamenepo Yesu anawayitana nawayankhula mʼmafanizo nati: “Kodi Satana angatulutse bwanji Satana?
I dozvavši ih govoraše im u prièama: kako može sotona sotonu izgoniti?
24 Ngati ufumu ugawanikana mwa iwo okha, ufumu umenewo sungakhalitse.
I ako se carstvo samo po sebi razdijeli, ne može ostati carstvo ono;
25 Ngati nyumba igawanikana mwa iyo yokha, nyumba imeneyo singathe kuyima.
I ako se dom sam po sebi razdijeli, ne može ostati dom onaj;
26 Ndipo ngati Satana adzitsutsa yekha sangathe kuyima; ulamuliro wake watha.
I ako sotona ustane sam na se i razdijeli se, ne može ostati, nego æe propasti.
27 Kunena zoona, palibe munthu angalowe mʼnyumba ya munthu wamphamvu ndi kutenga katundu wake pokhapokha atayamba wamumanga munthu wamphamvuyo. Pamenepo akhoza kumubera.
Niko ne može pokuæstvo jakoga, ušavši u kuæu njegovu, oteti ako najprije jakoga ne sveže: i onda æe kuæu njegovu oplijeniti.
28 Ndikukuwuzani zoona kuti machimo onse ndi zamwano zonse za anthu zidzakhululukidwa,
Zaista vam kažem: svi grijesi oprostiæe se sinovima èovjeèijim, i huljenja na Boga, makar kakova bila:
29 koma aliyense amene achitira mwano Mzimu Woyera sadzakhululukidwa pakuti wachita tchimo losatha.” (aiōn g165, aiōnios g166)
A koji pohuli na Duha svetoga nema oproštenja vavijek, nego je kriv vjeènome sudu. (aiōn g165, aiōnios g166)
30 Ananena izi chifukwa anati, “Ali ndi mzimu woyipa.”
Jer govorahu: u njemu je neèisti duh.
31 Pamenepo amayi ndi abale ake a Yesu anafika. Atayima kunja, anatuma wina kuti akamuyitane Iye.
I doðe mati njegova i braæa njegova, i stojeæi napolju poslaše k njemu da ga zovu.
32 Gulu la anthu linakhala momuzungulira Iye, ndipo anamuwuza kuti, “Amayi ndi abale anu ali panja akukufunani.”
I sjeðaše narod oko njega. I rekoše mu: eto mati tvoja i braæa tvoja i sestre tvoje napolju pitaju za te.
33 Iye anafunsa kuti, “Amayi ndi abale anga ndi ndani?”
I odgovori im govoreæi: ko je mati moja ili braæa moja?
34 Pamenepo anayangʼana anthu amene anakhala momuzungurira ndipo anati, “Awa ndi amayi anga ndi abale anga!
I pogledavši oko sebe na narod koji sjeðaše reèe: evo mati moja i braæa moja.
35 Aliyense amene achita chifuniro cha Mulungu ndi mʼbale wanga ndi mlongo wanga ndi amayi anga.”
Jer ko izvrši volju Božiju onaj je brat moj i sestra moja i mati moja.

< Marko 3 >