< Marko 16 >

1 Litapita tsiku la Sabata, Mariya Magadalena, ndi amayi ake a Yakobo, ndi Salome anagula zonunkhiritsa ndi cholinga chakuti apite akadzoze thupi la Yesu.
Sanbatay adhidappe guye Magidale Marama Yaqobe aayo Maramira Salomira issippe bidi Yesusa anha tiyanas shito shamida.
2 Mmamawa, tsiku loyamba la Sabata, dzuwa litangotuluka kumene, anali pa ulendo wopita ku manda
Samintafe koyro galas malado wontara buro awa arshey kezida mala Yesusa dufokk buro bishin
3 ndipo anafunsana wina ndi mnzake kuti, “Kodi akatikugudubuzira mwala pa khomo la manda ndani?”
“Dufoza dunappe shucha nuss ooni gendersanee?” gidi ba garsan hasa7etida.
4 Koma atakweza maso awo, anaona kuti mwala umene unali waukulu kwambiri wagubuduzidwa kale.
Issti dhoqu gi xelishin daro gitta shuchay dufoza dunappe genderidaysa beyida.
5 Atalowa mʼmanda, anaona mnyamata atavala mwinjiro woyera atakhala ku mbali ya kumanja, ndipo iwo anachita mantha.
Gede dufoza giddo gelida mala issi botha mayo mayida panthi ushacha bagara utidaysa beyidi dagamida.
6 Iye anati, “Musaope. Kodi mukufuna Yesu wa ku Nazareti, amene anapachikidwa? Wauka! Sali muno. Onani malo amene anamugonekapo.
Izi qass istas “Dagamopitte inte kaqetida Nazirete Yesusa koyista, izi dendidees han deena, issti iza wothidaso hayssa beyte” gidees.
7 Koma pitani, kawuzeni ophunzira ake ndi Petro kuti, ‘Iye watsogola kupita ku Galileya. Kumeneko mukamuona Iye monga momwe anakuwuzirani.’”
Gido atin inte biidi iza kalizaytasine Phixirosas kasse intes yotida mala inteppe kasetidi izi Galila bana. Inte iza hen demana gidi istas yotitte gidees.
8 Akunjenjemera ndi kudabwa, amayiwo anatuluka ndipo anathawa ku mandako. Sananene china chilichonse kwa aliyense, chifukwa anachita mantha.
Macashatikka malaletishene kokorishe dufappe kezi baqatida. Babida gish oonasikka aykkokka qatibeytena.
9 (note: The most reliable and earliest manuscripts do not include Mark 16:9-20.) Yesu atauka kwa akufa mmawa pa tsiku loyamba la Sabata, anayamba kuonekera kwa Mariya Magadalena, amene anatulutsa mwa iye ziwanda zisanu ndi ziwiri.
(note: The most reliable and earliest manuscripts do not include Mark 16:9-20.) Samintappe koyro galas Wogga wonta maladora izi hayqoppe dendidappe guye Yesusay izippe lappun daydanth kesida Magidale Maramis koyro betides.
10 Iye anapita ndi kukawawuza amene anali ndi Yesu, amene ankakhuza maliro ndi kulira.
Izakka bada kasse izara dizayti muzotishenne yekishe dishin demada yotadus.
11 Atamva kuti Yesu ali moyo ndikuti amuona, iwo sanakhulupirire.
Isti Yesusay paxa dizaysanne iza ta iza beyadis gidaysa siyidi amanibeytena.
12 Zitatha izi Yesu anaonekera mʼmaonekedwe ena kwa awiri a iwo amene anali ku dera la ku mudzi.
Hessappe guye iza kalizaytappe namm7ati gede dere gars bishin Yesusay isstas hara ass milati betidees.
13 Iwo anabwerera ndi kudzawawuza enawo; koma iwo sanakhulupirirebe.
Isstikka simidi hessa iza kalizaytappe atidaytas yotida. Gido atin iza kalizyti siyidi amaibeytena.
14 Pambuyo pake Yesu anaonekera kwa khumi ndi mmodziwo pamene ankadya; anawadzudzula chifukwa chopanda chikhulupiriro ndi kukanitsitsa kwawo kuti akhulupirire amene anamuona Iye atauka.
Hessappe guye tammane issineti kaththa madan dishin Yesusay istas qoncidees. Izi hayqoppe dendin iza beyida asati isstas yotin siyidi ammanonita agida gish isstas ammanoy bayndaysanne issta wozina mumetetha gish issta borides.
15 Anati kwa iwo, “Pitani mʼdziko lonse lapansi ndipo mukalalikire Uthenga Wabwino kwa zolengedwa zonse.
Isstaskka hizgidees “Gede alame wursoso biite, mishracho qaala medhetetha wursoso sabakitte.”
16 Aliyense amene akakhulupirire nabatizidwa adzapulumuka, koma amene sakakhulupirira adzalangidwa.
Aamanidayne xamaqetiday atana. Amanontay gidikko pirdistana.
17 Tsono zizindikiro izi zidzawatsata amene adzakhulupirira: Mʼdzina langa adzatulutsa ziwanda; adzayankhula malilime atsopano;
Tana amanizayta hayti malatati kalana. Isti ta sunthan daydanthata kesana, ooratha qalankka hasa7ana.
18 adzanyamula njoka ndi manja awo; ndipo pamene adzamwa mankhwala akupha, sadzawapweteka nʼpangʼonongʼono pomwe; adzasanjika manja awo pa anthu odwala ndipo odwalawo adzachira.”
Issti shoshata ba kushera oykkana, wodhiza marzekka uyikoka issta qohena. Be kushe harganchata bolla wothi wossikko haraganchati paxana.
19 Ambuye Yesu atatha kuyankhulana nawo, anatengedwa kupita kumwamba ndipo anakhala kudzanja lamanja la Mulungu.
Goda Yesusay hessa yotidappe gueye pudde salo dendidi bidi Xoossa ushacan utidees.
20 Pamenepo ophunzira aja anapita ndi kukalalikira ponseponse, ndipo Ambuye anagwira nawo ntchito pamodzi, ndipo anatsimikizira mawuwo ndi zizindikiro zimene ankachita.
Iza kalizayti hessappe kezidi wursoson adhi adhi sabakida. Godaykka isstara oothidees. Issta timirteza ekidi oothizaytas ba yotida qalakka malata othi othi minthidees.

< Marko 16 >