< Marko 13 >

1 Iye atachoka mʼNyumba ya Mulungu, mmodzi wa ophunzira ake anati kwa Iye, “Aphunzitsi taonani! Miyala ikuluikulu! Nyumba zikongolerenji!”
Ie niavotse i Anjomban’ Añaharey, le hoe ty mpiama’e raike: O Rañandria, anh’a anh’a! hehek’ o vato jabajabao, o anjomba fanjàkao!
2 Yesu anayankha kuti, “Kodi mukuziona nyumba zikuluzikuluzi? Palibe mwala ndi umodzi pano umene udzakhala pa unzake; uliwonse udzagwetsedwa pansi.”
Tinoi’ Iesoà ty hoe: Isa’o hao o anjomba fanjàka roañeo? Leo vato’e raike tsy hapoke ambone’ ty ila’e ze tsy hafetsake ambane.
3 Yesu atakhala pansi pa phiri la Olivi moyangʼanana ndi Nyumba ya Mulungu, Petro, Yakobo, Yohane ndi Andreya anamufunsa Iye pambali kuti,
Ie niambesatse am-bohi-Oliva, tandrife i Anjomban’ Añaharey, le natola’ i Petera naho Iakobe naho i Jaona naho i Andrea vaho nañontanea’ iareo ty hoe:
4 “Tatiwuzani, izi zidzachitika liti? Nanga chizindikiro chakuti zatsala pangʼono kukwaniritsidwa chidzakhala chiyani?”
Atalilio: ombia te ho tondroke o raha zao? Inoñe ty ho viloñe t’ie ho heneke?
5 Yesu anawawuza kuti, “Chenjerani kuti wina asakunyengeni.
Le namototse nitalily am’iareo ty hoe t’Iesoà: Mitaoa tsy ho verevereñe;
6 Anthu ambiri adzabwera mʼdzina langa, nadzati, ‘Ine ndi Iyeyo,’ ndipo adzanamiza anthu ambiri.
maro ty hiboak’ ami’ty añarako hanao ty hoe, Izaho ro ie, hampandifike ty maro.
7 Pamene mudzamva zankhondo ndi mbiri zankhondo, musadzadzidzimuke. Zinthu zotere ziyenera kuchitika, koma sikuti chimaliziro chafika kale ayi.
Le ie janji’ areo amo ali-taneo naho o talilin’ alio, ko mahimahiñe, amy t’ie tsy mete tsy ho avy, fe mbe tsy ie i figadoñañey.
8 Mtundu udzawukira mtundu unzake, ndi ufumu kuwukira ufumu unzake. Kudzakhala zivomerezi mʼmalo osiyanasiyana, ndi njala. Izi ndi chiyambi chabe cha zowawa monga mayi pobereka.
Hiongake hifañatreatre ami’ty fifelehañe ty fifelehañe, naho ami’ty fifeheañe ty fifeheañe, naho hiezeñezeñe ty tane ila’e añe, vaho ho paohe’ ty hasalikoañe; ty fifotoram-pitsongoan’ ampela avao irezay.
9 “Muyenera kukhala tcheru. Mudzaperekedwa ku mabwalo oweruza ndi kukwapulidwa mwankhanza mʼmasunagoge. Mudzayima pamaso pa abwanamkubwa ndi mafumu monga mboni kwa iwo chifukwa cha Ine.
Aa le mitaoa, fa hasese’ iereo am-pivory ao, naho ho fofoheñe am-pitontonañ’ ao, vaho hajohañe añatrefam-pandily naho mpanjaka eo ty amako ho fitaliliañe ama’e.
10 Ndipo Uthenga Wabwino uyenera kuyamba walalikidwa kwa anthu a mitundu yonse.
Fa tsy mete tsy taroñeñe amy ze kilakila ondaty hey i talili-soay.
11 Nthawi iliyonse pamene mwamangidwa ndi kuyimbidwa mlandu, musadandaule za zimene mudzanena. Zimene mudzapatsidwe pa nthawiyo yankhulani; pakuti sindinu amene mudzayankhula, koma Mzimu Woyera.
Aa ie tantalieñe naho seseheñe, ko mimenomenoñe amy ze ho saontsie’ areo, le ko mañereñere aolo; fe saontsio ze hatolotse amy ora zay, amy te tsy inahareo ty hisaontsy, fa i Arofo Masiñey.
12 “Mʼbale adzapereka mʼbale kuti aphedwe, ndipo abambo adzapereka mwana wawo. Ana adzawukira makolo awo ndi kuwapereka kuti aphedwe.
Hasesen-drahalahy ty rahalahi’e havetrake, le ty rae i ana’e, naho hiongake aman-droae’e o ana’eo hañoho-doza ama’e.
13 Anthu onse adzakudani chifukwa cha Ine, koma amene adzalimbika mpaka potsiriza, ameneyo ndiye adzapulumuke.
Kila halaiñe anahareo ty ami’ty añarako, fe ho rombaheñe ty mahafeake pak’ am-para’e.
14 “Mukadzaona ‘chinthu chonyansa chosakaza’ chitayima pa malo amene si ake, owerenga azindikire. Pamenepo amene ali ku Yudeya athawire kumapiri.
Aa naho vazoho’ areo mijagaro­doñe amy tsy mete ijohañañey ty Hativà’ o Fandrotsahañeo, (ehe te mahaoniñe ty mpamaky); le mihere­reaha an-day mb’ am-bohitse mb’eo ze hene e Iehodà ao;
15 Aliyense amene ali pa denga la nyumba yake asatsike kapena kulowa mʼnyumba kukatenga kanthu kalikonse.
Asoao tsy hizotso ty ambone’ anjomba eo himoake añ’akiba ao hañakatse raha.
16 Aliyense amene ali ku munda asabwerere kukatenga mkanjo wake.
Asoao tsy hibalike handrambe ty sarimbo’e ze an-teteke añe.
17 Kudzakhala koopsa mʼmasiku amenewo kwa amayi oyembekezera ndi amayi oyamwitsa!
Feh’ ohatse ho amo mivesatse naho mampinono amy andro rezaio!
18 Pempherani kuti zimenezi zisadzachitike nthawi yozizira,
Le mihalalia te tsy ho ami’ty asotry ty hifetsaha’e.
19 chifukwa masiku amenewo adzakhala owawitsa osafanana ndi ena kuyambira pachiyambi, pamene Mulungu analenga dziko, kufikira lero ndipo sadzafanananso ndi ena.
Fa ho sam-poheke mboe tsy nizoeñe an-tane atoy sikal’ ami’ty fifotora’ ty voatse namboaren’ Añahare toy pake henane vaho tsy ho ama’e ka—i andro rezay.
20 Ambuye akanapanda kufupikitsa masikuwo, palibe amene akanapulumuka. Koma chifukwa cha osankhidwiratu, amene anawasankha, Iye anawafupikitsa.
Aa naho tsy nampitomots’ andro t’i Talè, le tsy ho nitendreke nofotse ho rombaheñe; fe o noro’e jinobo’eo ro naña­tomora’e i andro rey.
21 Pa nthawi imeneyo, ngati wina adzati kwa inu, ‘Taonani, Khristu ali kuno, kapena, Taonani, uyo ali apoyo!’ musakhulupirire.
Ie amy zao, naho eo ty hanao ama’ areo ty hoe: Hehe, ingo i Norizañey; naho, Hehe, inge! Ko miantoke,
22 Pakuti akhristu onama ndi aneneri onama adzaonekera ndipo adzachita zizindikiro ndi zodabwitsa kuti anyenge osankhidwiratu ngati kutakhala kotheka kutero.
amy te hiongake o norizam-bìlañeo, naho o mpitoky sare’eo, hampiboake viloñe vaho halatsàñe han­drantoa’e o jinoboñeo naho ho nimete.
23 Choncho khalani tcheru; ndakuwuzani zonse nthawi isanafike.
Aa le itaò: Ingo fa hene nataliliko ama’areo aolo.
24 “Koma masiku amenewo, masautsowo atatha, “‘dzuwa lidzada, ndipo mwezi sudzawala;
Ie amy andro rezay, naho fa añe i san-kaemberañey, le hampaieñeñe i àndroy, naho tsy hañomey ty hazavà’e i volañey,
25 nyenyezi zidzagwa kuchokera ku thambo, ndipo mayiko mumlengalenga adzagwedezeka!’
naho hirarake o vasian-dikerañeo, vaho ho ozoñozòñeñe o haozarañe andindìñeo.
26 “Nthawi imeneyo anthu adzaona Mwana wa Munthu akubwera mʼmitambo ndi mphamvu yayikulu ndi ulemerero.
Vaho ho isa’ iereo mitotsake amo rahoñeo ey an-kaozarañe naho engeñe ra’elahy i Ana’ Ondatiy.
27 Ndipo adzatuma angelo ake kukasonkhanitsa osankhidwiratu ake ku mphepo zinayi, kuyambira kumalekezero a dziko lapansi mpaka ku malekezero ake enanso.
Le hahitri’e mb’eo o anjeli’eo, hanontoñe o jinobo’eo boak’ami’ty fihirifa’ o tiok’ efatseo, sikala añ’ olo’ ty tane toy añe pak’ añ’ indran-dikerañe añe.
28 “Tsopano phunzirani phunziro ili kuchokera ku mtengo wamkuyu. Pamene msonga za nthambi zake zikhala za nthete ndipo masamba ake ayamba kuphukira, mumadziwa kuti dzinja layandikira.
Rendreho ty razañe’ o sakoañeo: Ie fa maleme ty lengo’e, naho mibotiboty o rave’eo, le fohi’ areo te miha-asara ty taoñe.
29 Momwenso pamene muona zinthu izi zikuchitika, dziwani kuti wayandikira, ali pa khomo.
Hoe izay ka nahareo, ie maharendreke ty fifetsaha’ irezay; fohino te mitotoke, vaho fa an-dalam-bey eo.
30 Zoonadi, Ine ndikuwuzani kuti mʼbado uno sudzatha mpaka zinthu zonsezi zitachitika.
Eka! to t’itaroñako te tsy himosaoñe añe ty fifokoañe toy naho tsy tendreke hey irezay.
31 Kumwamba ndi dziko lapansi zidzatha, koma mawu anga sadzatha.”
Hisaok’ añe i likerañey naho ty tane toy, fa tsy hihelañe ka o volakoo.
32 “Palibe amene akudziwa za tsikulo kapena nthawi, ngakhale angelo akumwamba, kapena Mwana, koma Atate wokha.
Aa ty amy àndroy naho i ora zay, tsy ia ty mahafohiñe ndra o anjely andindìñeo ndra i Anakey, fa t’i Rae avao.
33 Khalani maso! Khalani tcheru! Simudziwa pamene nthawi imeneyo idzafike.
Mitaoa, mijilova; amy te tsy fohi’ areo ty hitondroha’ i àndroy.
34 Zili ngati munthu amene akuchokapo. Amasiyira nyumba yake antchito ake, aliyense ndi ntchito yake; ndi kumuwuza wa pa khomo kuti azikhala maso.
Razañeñe amy t’indaty nañavelo añe; ie nienga ty anjomba’e, naho tinolo’e lily o mpitoro’eo, naho songa nizarae’e fitoloñañe, vaho namantok’ amy mpigarin-dalambeiy te hijilojilo.
35 “Inunso muyenera kukhala maso chifukwa simukudziwa nthawi imene mwini nyumba adzabwere, kaya madzulo, kapena pakati pa usiku, kapena tambala akulira, kapena mʼbandakucha.
Aa le mitaòa, amy te tsy fohi’ areo ty hibaliha’ i talèn’ anjombay, ke hariva, he antets’ale, kera amy kekeon-akohoy, hera maraindray;
36 Ngati atabwera mwadzidzidzi, asadzakupezeni inu muli mtulo.
tsy mone hitojeha re hanjò anahareo mirotse.
37 Zimene ndikunena kwa inu, ndikunena kwa aliyense: ‘Khalani tcheru!’”
O itaroñakoo ro taroñeko amy ze hene ondaty: Mitaoa!

< Marko 13 >