< Marko 11 >
1 Atayandikira ku Yerusalemu, anafika ku Betifage ndi Betaniya ku phiri la Olivi. Yesu anatuma awiri a ophunzira ake
Když se blížili k Jeruzalému a stoupali na Olivovou horu, uviděli Betfage a Betanii. Ježíš poslal dva ze svých učedníků napřed
2 nati kwa iwo, “Pitani ku mudzi uli patsogolo panu, ndipo mukamakalowa, mukapeza mwana wabulu atamangiriridwa pamenepo, amene wina aliyense sanakwerepo. Kamumasuleni ndi kubwera naye kuno.
a řekl jim: „Jděte do vesnice tamhle před námi. Na kraji vesnice uvidíte u plotu uvázané oslátko, na kterém ještě nikdo nejel. To mi přiveďte.
3 Ngati wina aliyense akakufunsani kuti, ‘Mukuchita zimenezi chifukwa chiyani?’ Kamuwuzeni kuti, ‘Ambuye akumufuna ndipo akamutumiza kuno msanga.’”
A kdyby se vás někdo ptal, co to děláte, odpovězte krátce: Pán ho potřebuje a brzy ho vrátí.“
4 Anapita ndipo anakapeza mwana wabulu ali kunja mu msewu waukulu atamumangirira pa chipata. Pamene anamumasula,
Učedníci šli a skutečně našli u jednoho domu přivázané oslátko.
5 anthu ena amene anayima pomwepo anafunsa kuti, “Mukuchita chiyani, kumasula mwana wabuluyo?”
Když ho odvazovali, někteří z kolemjdoucích se ptali, proč to dělají.
6 Iwo anayankha monga mmene Yesu anawawuzira, ndipo anthu aja anawalola kuti apite.
Odpověděli tak, jak jim poradil Ježíš, a lidé je nechali zvíře odvést.
7 Atafika naye mwana wabulu kwa Yesu, nayika mikanjo yawo pa buluyo, Iye anakwerapo.
Přivedli oslátko k Ježíšovi, přehodili přes ně své pláště, Ježíš se na ně posadil a vydali se na cestu.
8 Anthu ambiri anayala mikanjo yawo pa msewu, pamene ena anayala nthambi zomwe anadula mʼminda.
Lidé ze zástupu, který ho provázel, se začali předhánět v pozornostech; prostírali před ním své pláště, jiní lámali větve a zdobili jimi cestu.
9 Amene anatsogola ndi iwo amene ankatsatira ankafuwula kuti, “Hosana! “Odala Iye amene akudza mʼdzina la Ambuye!”
Za ním i před ním se utvořil průvod a všichni volali: „Ať žije král! Sláva!
10 “Odala ndi ufumu umene ukubwera wa abambo athu Davide!” “Hosana Mmwambamwamba!”
Jde v Božím jménu! Ať žije Davidovo království! Nebe jásá s námi!“
11 Yesu analowa mu Yerusalemu napita ku Nyumba ya Mulungu. Anayangʼana zonse, koma popeza kuti nthawi inali itapita, anatuluka kupita ku Betaniya pamodzi ndi khumi ndi awiriwo.
Tak vstoupil Ježíš do Jeruzaléma a vešel do chrámu. Všechno si tam pozorně prohlédl, a protože byl již večer, odešel se svými dvanácti na noc do Betanie.
12 Mmawa mwake pamene amachoka ku Betaniya, Yesu anamva njala.
Druhý den cestou z Betanie dostal Ježíš hlad.
13 Ataonera patali mtengo wamkuyu uli ndi masamba, anapita kuti akaone ngati unali ndi chipatso chilichonse. Atafika, sanapezemo kanthu koma masamba, chifukwa sinali nthawi ya nkhuyu.
Z dálky uviděl fíkovník obalený listím a šel se podívat, zda nemá nějaké ovoce. Když pak přišel až ke stromu, zjistil, že kromě listí na něm nic neroste; první úroda byla pryč a na novou strom ještě nenasadil.
14 Ndipo Iye anati kwa mtengo, “Palibe amene adzadyenso chipatso kuchokera kwa iwe.” Ndipo ophunzira ake anamva Iye akunena izi. (aiōn )
Učedníci slyšeli, jak říká stromu: „Nikdo už z tebe nebude jíst ovoce!“ (aiōn )
15 Atafika ku Yerusalemu, Yesu analowa mʼbwalo lakunja la Nyumba ya Mulungu ndipo anayamba kupirikitsa anthu amene amagula ndi kugulitsa mʼmenemo. Anagubuduza matebulo a osintha ndalama ndi mipando ya ogulitsa nkhunda,
Vrátili se do Jeruzaléma a Ježíš šel do chrámu. Když na nádvoří chrámu uviděl stánky s obětními zvířaty a pulty směnárníků, zpřevracel je a obchodníky vyhnal.
16 ndipo Iye sanalole aliyense kugulitsa malonda mʼmabwalo a Nyumba ya Mulungu.
Nedovolil ani, aby si někdo tamtudy krátil cestu s vodou od studny.
17 Ndipo pamene ankawaphunzitsa, Iye anati, “Kodi sikunalembedwe kuti, ‘Nyumba yanga idzatchedwa Nyumba ya mapemphero kwa anthu a mitundu yonse?’ Koma inu mwayisandutsa ‘phanga la achifwamba.’”
„Cožpak nevíte, “horlil, „že je napsáno v Písmu: ‚Můj chrám je určen k tomu, aby se v něm všechny národy modlily?‘Vy jste však z něho udělali lupičské doupě.“
18 Akulu a ansembe ndi aphunzitsi amalamulo anamva izi ndipo anayamba kufuna njira yoti amuphere Iye, pakuti amamuopa, chifukwa gulu lonse la anthu linazizwa ndi chiphunzitso chake.
Slyšeli to i velekněží a učitelé zákona a přemýšleli, jak by se Ježíše zbavili. Měli z něho strach, protože lid byl jeho učením nadšen.
19 Pofika madzulo, iwo anatuluka mu mzindamo.
Večer Ježíš s učedníky opustil město.
20 Mmamawa, pamene ankayenda, anaona mtengo wamkuyu uja utafota kuyambira ku mizu.
Když šli ráno zase kolem toho fíkovníku, viděli, že je úplně suchý.
21 Petro anakumbukira nati kwa Yesu, “Aphunzitsi, taonani! Mtengo wamkuyu munawutemberera uja wafota!”
Petr si vzpomněl na včerejší příhodu. „Mistře, ten fíkovník, který jsi odsoudil, uschl!“
22 Yesu anayankha kuti, “Khalani ndi chikhulupiriro mwa Mulungu.
„To vás překvapuje?“usmál se Ježíš. „Boží moc je daleko větší.
23 Zoonadi, Ine ndikuwuzani kuti ngati wina aliyense angalamule phiri ili kuti, ‘Pita, kadziponye mʼnyanja,’ ndipo wosakayika mu mtima mwake koma kukhulupirira kuti chimene akunena chidzachitika, chidzachitikadi kwa iyeyo.
Když budete věřit Bohu – a myslím to smrtelně vážně – a řekli byste této hoře: ‚Zvedni se a padni do moře, ‘ta hora to udělá. Musíte jen věřit bez nejmenší pochybnosti.
24 Nʼchifukwa chake ndikukuwuzani kuti chilichonse chimene mupempha mʼpemphero, khulupirirani kuti mwalandira, ndipo chidzakhala chanu.
Pamatujte si: budete-li za něco prosit ve svých modlitbách s pevnou vírou, že vaše prosba bude naplněna, pak se tak určitě stane.
25 Pamene muyimirira kupemphera, ngati muli ndi chifukwa ndi wina, mukhululukireni, kuti Atate anu akumwamba akukhululukireni machimo anu.”
Ale když se modlíte, odpusťte nejdříve tomu, proti komu něco máte, aby i váš nebeský Otec mohl odpustit vám.
26 (Koma ngati simukhululukirana, ngakhale Atate anu akumwamba sadzakhululukira machimo anu).
Jestliže ve vás zůstane hněv, ani Bůh vám nepromine vaše provinění.“
27 Iwo anafikanso ku Yerusalemu, ndipo pamene Yesu amayenda mʼmabwalo a Nyumba ya Mulungu, akulu a ansembe, aphunzitsi amalamulo ndi akuluakulu anabwera kwa Iye.
Přišli zase do Jeruzaléma. Když Ježíš procházel chrámem, zastavili ho zástupci představenstva chrámu
28 Iwo anafunsa kuti, “Mukuchita izi ndi ulamuliro wanji? Ndipo anakupatsani ulamuliro umenewu ndi ndani?”
„Od koho máš pověření k takovým činům? Kdo tě k tomu zmocnil?“
29 Yesu anayankha kuti, “Ndikufunsani funso limodzi. Mundiyankhe, ndipo ndikuwuzani ndi ulamuliro wanji umene ndikuchitira izi.
„Já se vás také zeptám na jednu věc, “opáčil Ježíš. „Když mi odpovíte, řeknu i já, od koho mám tu moc.
30 Ubatizo wa Yohane, unali wochokera kumwamba, kapena kwa anthu? Ndiwuzeni.”
Povězte mi: Byl Jan Křtitel skutečně poslán od Boha, nebo si to vymyslel?“
31 Iwo anakambirana pakati pawo ndipo anati, “Tikati, ‘Wochokera kumwamba,’ atifunsa kuti, ‘Nanga nʼchifukwa chiyani simunamukhulupirire?’
Dali hlavy dohromady: „Odpovíme-li, že od Boha, pak nám řekne, proč jsme mu tedy neuvěřili.
32 Koma ife tikati, ‘Wochokera kwa anthu.’” (Amaopa anthu, pakuti aliyense amakhulupirira kuti Yohane analidi mneneri).
A před lidmi zase nemůžeme Jana prohlásit za obyčejného fanatika. Vždyť jsou všichni přesvědčeni, že to byl Boží prorok.“
33 Ndipo anamuyankha Yesu kuti, “Sitikudziwa.” Yesu anati, “Nanenso sindikuwuzani kuti ndi ulamuliro wanji ndichitira zimenezi.”
A tak odpověděli Ježíšovi: „Nevíme!“„Ani já vám tedy nepovím, od koho mám pověření, “odtušil Ježíš.