< Malaki 4 >

1 Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Ndithu tsiku likubwera; lidzayaka ngati ngʼanjo. Anthu onse odzikuza, ndi aliyense ochita zoyipa adzapsa ngati chiputu, ndipo pa tsiku limene likubweralo adzapserera ndi moto. Sipadzatsalira muzu kapena nthambi.
Xəəne G'oşunbışde Rəbbee eyhen: – Peşt xhinne gyotxhanan yiğ k'ane qexhe vod. Gırgın cocab co axtıba vukkekanbıyiy pisvalla haa'anbı, mane yiğıl balybiy xhinne gyooxhanas. Mane k'ane qexhene yiğın manbı gyooxhan haa'asınbı. Manbışike kokbıd, bıtağbıd axvas deş.
2 Koma inu amene mumaopa dzina langa, dzuwa lachilungamo lidzakutulukirani lili ndi kuwala kokuchiritsani. Ndipo inu mudzatuluka ndi kulumphalumpha ngati ana angʼombe amene atulutsidwa mʼkhola.
Zale qəvəyq'ənanbışdemeeme, Qopkuvalina verığ ılqevç'es. Mançine şü'ülee yug qav'iy ixhes. Ağıleençe g'aykkiyn q'ıkar xhinne şu huvaagas.
3 Tsiku limenelo inu mudzapondereza anthu oyipa; adzakhala phulusa ku mapazi anu pa tsiku limene Ine ndidzachite zinthu zimenezi,” akutero Yehova Wamphamvuzonse.
Pisınbı şu kööq'əsınbı. Zı man ha'asde yiğıl, manbı vuşde g'elybışik avub yı'q xhinne vuxhes. Məxüd Xəəne G'oşunbışde Rəbbee eyhe!
4 Kumbukirani zophunzitsa za mtumiki wanga Mose, malamulo ndi malangizo amene ndinamupatsa pa Horebu kuti awuze Aisraeli onse.
Yizda nukar Mısa Xorevne suvalynang'a, Zı mang'us İzrailyne milletnemeecab huvuna Q'aanun, Yizın g'aydabıyiy əmrbı şu yik'el aqqe.
5 “Taonani, ndidzakutumizirani mneneri Eliya lisanafike tsiku lalikulu ndi loopsa la Yehova.
İlyaake, Rəbbin xədın, dağamın yiğ qalesse, Zı şosqa İlyas peyğambar g'axıles.
6 Iye adzabweza mitima ya makolo kwa ana awo, ndi mitima ya ana kwa makolo awo. Kupanda kutero ndidzabwera kudzakantha dziko lanu ndi temberero.”
Zı qarı in cigabı kunfa-yakun hıma'acenva, Mang'vee dekkaaşin yik'bı dixbışilqa, dixbışinbıd dekkaaşilqa sak'al ha'as.

< Malaki 4 >