< Malaki 4 >

1 Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Ndithu tsiku likubwera; lidzayaka ngati ngʼanjo. Anthu onse odzikuza, ndi aliyense ochita zoyipa adzapsa ngati chiputu, ndipo pa tsiku limene likubweralo adzapserera ndi moto. Sipadzatsalira muzu kapena nthambi.
Khohnin akapai tahhmaiulh bangla alh ngawn coeng he. Tedongah thinlen boeih neh halangnah akasaii boeih tahdivawt banglaom vetih khohnin akapai lohamih te a hlawp ni. Caempuei BOEIPA loh a thui bangla amih te a yung lamloh a hlaeng khawhnawt mahpawh.
2 Koma inu amene mumaopa dzina langa, dzuwa lachilungamo lidzakutulukirani lili ndi kuwala kokuchiritsani. Ndipo inu mudzatuluka ndi kulumphalumpha ngati ana angʼombe amene atulutsidwa mʼkhola.
Tedae ka ming akarhih nangmih ham tahduengnah khomik thoeng ni. Tevaengah a phae dongkah hoeihnah neh cet vetih tesael-im kahsaelca bangla napet uh ni.
3 Tsiku limenelo inu mudzapondereza anthu oyipa; adzakhala phulusa ku mapazi anu pa tsiku limene Ine ndidzachite zinthu zimenezi,” akutero Yehova Wamphamvuzonse.
“Ka saii khohnin ah tahhalang rhoek te naneet uh vetihna kho dongkahkhopha hmui ah hmaiphu la om ni,” tilacaempuei BOEIPA loh a thui.
4 Kumbukirani zophunzitsa za mtumiki wanga Mose, malamulo ndi malangizo amene ndinamupatsa pa Horebu kuti awuze Aisraeli onse.
Ka sal Moses kaholkhueng poek uh. Te teIsrael boeih kaholtlueh neh laitloeknah ham niHoreb ah anih te kauen.
5 “Taonani, ndidzakutumizirani mneneri Eliya lisanafike tsiku lalikulu ndi loopsa la Yehova.
BOEIPA kahrhihom khohnin puei a pai tom ah tonghma Elijah te nangmih taengla kan tueih coeng he.
6 Iye adzabweza mitima ya makolo kwa ana awo, ndi mitima ya ana kwa makolo awo. Kupanda kutero ndidzabwera kudzakantha dziko lanu ndi temberero.”
Tedongah pa rhoek kahlungbuei ca rhoektaengla, ca rhoek kahlungbuei a napa taengla a mael puei ni. Kacet tih khohmuen te yaehtaboeih la kangawn tarhave.

< Malaki 4 >