< Malaki 3 >

1 Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Ine ndidzatuma mthenga wanga amene adzakonza njira pamaso panga. Kenaka mwadzidzidzi Ambuye amene mukumufunafuna adzafika ku Nyumba yake. Mthenga wapangano amene mukumuyembekezera adzabwera.”
Så Jag vill utsända min Ängel, den der vägen rör mig bereda skall; och med hast skall komma till sitt tempel Herren, den I söken, och förbundsens Ängel, den I begären. Si, han kommer, säger Herren Zebaoth.
2 Koma ndani adzatha kupirira pa tsiku la kubwera kwake? Ndani adzatha kuyima pamene Iye wafika? Pakuti adzakhala ngati moto wa mmisiri wa pa ngʼanjo, kapenanso ngati sopo wa munthu wochapa.
Men ho kan lida hans tillkommelses dag? Och ho skall bestå, då han låter sig se? Ty han är lika som en guldsmeds eld, och såsom en vaskerskos såpa.
3 Iye adzachita kukhalira pansi ngati mmisiri woyenga ndi woyeretsa siliva. Iye adzayeretsa Alevi ndi kuwayenga ngati golide ndi siliva. Pamenepo Yehova adzakhala ndi anthu amene azidzabweretsa zopereka mwachilungamo,
Han skall sitta, och smälta och fäja silfret; han skall fäja och rensa Levi söner, lika som silfver och guld; Så skola de då offra spisoffer uti rättfärdighet Herranom.
4 ndipo Yehova adzalandira zopereka za Yuda ndi Yerusalemu, ngati masiku akale, masiku amakedzana.
Och Juda och Jerusalems spisoffer skall väl behaga Herranom, lika som fordomdags, och i de förra år.
5 Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Tsono ndidzakuyandikirani kuti ndikuweruzeni. Mosataya nthawi ndidzanena mawu otsutsa mfiti, achigololo, a umboni wonama, amene salipira bwino antchito awo, amene amazunza akazi ndi ana amasiye, amene saweruza alendo mwachilungamo, komanso amene sandiopa Ine.”
Och jag skall komma till eder, och straffa eder, och skall vara ett snart vittne emot de trollkarlar, horkarlar och menedare, och emot dem som vild och orätt göra dagakarlenom, enkone och dem faderlösa, och förtrycka främlingen, och intet frukta mig, säger Herren Zebaoth.
6 “Ine ndine Yehova, ndipo sindisintha. Choncho inu zidzukulu za Yakobo, simunawonongedwe.
Ty jag är Herren, den icke ljuger; och I, Jacobs barn, skolen icke allesamman förgås.
7 Kuyambira nthawi ya makolo anu mwakhala mukuphwanya malamulo anga ndipo simunawatsatire. Bwererani kwa Ine, ndipo Ine ndidzabwerera kwa inu,” akutero Yehova Wamphamvuzonse. “Koma inu mukufunsa kuti, ‘Tibwerere motani kwa Yehova?’
I hafven ifrå edra fäders tid allstädes afvikit ifrå min bud, och intet hållit dem. Så omvänder eder nu till mig, så vill lag ock vända mig till eder, säger Herren Zebaoth. Så sägen I då: Hvarutinnan skole vi omvända oss?
8 “Kodi munthu angathe kuba za Mulungu? Komatu inu mumandibera. “Koma inu mukufunsa kuti, ‘Kodi timakuberani motani?’ “Pa zakhumi ndi pa zopereka.
Är det rätt, att en menniska besviker Gud, såsom I besviken mig? Så sägen I då: Hvarmed besvike vi dig? Med tiond och häfoffer.
9 Mtundu wanu wonse ndinu otembereredwa, chifukwa mukundibera.
Derföre ären I ock förbannade, så att all ting försvinner eder undan händerna; ty I besviken mig allesamman.
10 Bweretsani chakhumi chathunthu ku nyumba yosungira, kuti mukhale chakudya mʼnyumba mwanga.” Akutero Yehova Wamphamvuzonse, “Tandiyesani, ndipo muone ngati sindidzatsekula zipata zakumwamba, ndi kukugwetserani madalitso ochuluka amene mudzasowe malo owayikamo.
Men förer mig tiondena allesammans uti mina tiondelado, att i mino huse må spis vara; och bepröfver mig härutinnan, säger Herren Zebaoth, om jag ock icke upplåter eder himmelens fenster, och gjuter välsignelse neder tillfyllest.
11 Ndidzaletsa tizirombo kuti tisawononge mbewu zanu, ndipo mpesa wa mʼminda mwanu zipatso zake sizidzayoyoka,” akutero Yehova Wamphamvuzonse.
Och jag vill för eder straffa frätaren att han icke skall förderfva fruktena på markene, och att vinträt i åkrenom icke skall vara eder ofruktsamt, säger Herren Zebaoth;
12 “Motero anthu amitundu yonse adzakutchulani odala, pakuti dziko lanu lidzakhala lokondweretsa,” akutero Yehova Wamphamvuzonse.
Så att alle Hedningar skola prisa eder saliga; ty I skolen vara ett kosteligit land, säger Herren Zebaoth.
13 Yehova akuti, “Mwayankhula mawu owawa onena za Ine. “Komabe inu mukufunsa kuti, ‘Kodi tanena chiyani chotsutsana nanu?’
I talen hårdeliga emot mig, säger Herren. Så sägen I då: Hvad tale vi emot dig?
14 “Mwanena kuti, ‘Kutumikira Mulungu nʼkosapindulitsa. Kodi timapindulanji pochita zofuna zake, ndi kumayenda ngati anamfedwa pamaso pa Yehova Wamphamvuzonse?
Dermed, att I sägen: Det är förgäfves, att man Gudi tjenar, och hvad båtar det, att vi hållom hans bud, och förom ett strängt lefverne för Herranom Zebaoth?
15 Koma tsono ife timati anthu odzikuza ndiye odalitsika. Kunena zoona anthu oyipa ndiye amapeza bwino, ngakhale amene amanyoza Mulungu amapulumuka.’”
Derföre prise vi de föraktare; ty de ogudaktige växa till; de försöka Gud, och det går dem alltsammans väl utaf.
16 Ndipo woopa Yehova anayamba kukambirana, ndipo Yehova anamvetsera. Buku la chikumbutso linalembedwa pamaso pake, lonena za amene amaopa Yehova ndi kulemekeza dzina lake.
Men de, som frukta Herran, trösta hvarann alltså: Herren märker det, och hörer det; och det är en tänkeskrift för honom skrifven, för dem som frukta Herran, och tänka uppå hans Namn.
17 Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Anthu amenewo adzakhala anga, tsiku limene Ine ndidzachita izi, adzakhala angaanga. Ndidzawaleka osawalanga monga mmene munthu amachitira chifundo mwana wake amene amamutumikira.
De skola, säger Herren Zebaoth, vara min egendom på dem dagenom, den jag göra skall; och jag vill skona dem, lika som man skonar sin egen son, den honom tjenar.
18 Pamenepo mudzaonanso kusiyana pakati pa anthu olungama ndi oyipa, pakati pa amene amatumikira Mulungu ndi amene satumikira Mulungu.”
Och I skolen deremot åter se, hvad för en åtskilnad är emellan den rättfärdiga och den ogudaktiga, och emellan den som Gudi tjenar, och den som honom icke tjenar.

< Malaki 3 >