< Malaki 3 >

1 Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Ine ndidzatuma mthenga wanga amene adzakonza njira pamaso panga. Kenaka mwadzidzidzi Ambuye amene mukumufunafuna adzafika ku Nyumba yake. Mthenga wapangano amene mukumuyembekezera adzabwera.”
“Neuru, abiro oro jaotena mabiro losona yo kapok abiro. Bangʼe, apoya nono Ruoth mudwarono nobi e hekalune; jaote mar singruok, ma ugombo, nobi,” Jehova Nyasaye Maratego owacho.
2 Koma ndani adzatha kupirira pa tsiku la kubwera kwake? Ndani adzatha kuyima pamene Iye wafika? Pakuti adzakhala ngati moto wa mmisiri wa pa ngʼanjo, kapenanso ngati sopo wa munthu wochapa.
To en ngʼa manyalo siro chiengʼ biro mare? Koso en ngʼa manyalo chungʼ e nyime ka othinyore? Nimar enobed kaka mach mar jatheth kata sabund jaluoko malwoko maler.
3 Iye adzachita kukhalira pansi ngati mmisiri woyenga ndi woyeretsa siliva. Iye adzayeretsa Alevi ndi kuwayenga ngati golide ndi siliva. Pamenepo Yehova adzakhala ndi anthu amene azidzabweretsa zopereka mwachilungamo,
Nobed piny kaka jachung kendo japwodh fedha; nopwodh jo-Lawi kendo nochung-gi mana ka dhahabu gi fedha. Bangʼe Jehova Nyasaye nobedi gi joma kare manokelne chiwo,
4 ndipo Yehova adzalandira zopereka za Yuda ndi Yerusalemu, ngati masiku akale, masiku amakedzana.
kendo Jehova Nyasaye norwak chiwo mag Juda kod Jerusalem mana kaka ndalo mokadho.
5 Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Tsono ndidzakuyandikirani kuti ndikuweruzeni. Mosataya nthawi ndidzanena mawu otsutsa mfiti, achigololo, a umboni wonama, amene salipira bwino antchito awo, amene amazunza akazi ndi ana amasiye, amene saweruza alendo mwachilungamo, komanso amene sandiopa Ine.”
Jehova Nyasaye Maratego wacho niya, “Omiyo abiro sudo machiegni kodu mondo angʼadnu bura, anabi mapiyo mondo abed janeno ka kwedo ajuoke, jochode kod jogo makwongʼore kariambo, joma mayo jotijegi e yor chudo, jogo matimo marach ne mon ma chwogi otho kod nyithind kiye, kod jogo matamo jodak e adiera margi, nikech ok giluora.”
6 “Ine ndine Yehova, ndipo sindisintha. Choncho inu zidzukulu za Yakobo, simunawonongedwe.
Jehova Nyasaye Maratego wacho niya, “An Jehova Nyasaye ok alokra ngangʼ. Omiyo un, yaye nyikwa Jakobo, ok osetieku.
7 Kuyambira nthawi ya makolo anu mwakhala mukuphwanya malamulo anga ndipo simunawatsatire. Bwererani kwa Ine, ndipo Ine ndidzabwerera kwa inu,” akutero Yehova Wamphamvuzonse. “Koma inu mukufunsa kuti, ‘Tibwerere motani kwa Yehova?’
Nyaka chakre ndalo kwereu uselokoru uweyo yorega, kendo pok uritogi. Dwoguru ira to anaduog iru.” “To upenjo ni, ‘Ere kaka dwaduog iri?’
8 “Kodi munthu angathe kuba za Mulungu? Komatu inu mumandibera. “Koma inu mukufunsa kuti, ‘Kodi timakuberani motani?’ “Pa zakhumi ndi pa zopereka.
“Bende dhano nyalo mayo Nyasaye? To kata kamano, umaya. “Umedo penjo ni, ‘Kare ere kaka wamayi?’ “Umaya kuom chiwo mar achiel kuom apar kod chiwo mamoko.
9 Mtundu wanu wonse ndinu otembereredwa, chifukwa mukundibera.
Okwongʼ, ogandau duto, nikech umaya.”
10 Bweretsani chakhumi chathunthu ku nyumba yosungira, kuti mukhale chakudya mʼnyumba mwanga.” Akutero Yehova Wamphamvuzonse, “Tandiyesani, ndipo muone ngati sindidzatsekula zipata zakumwamba, ndi kukugwetserani madalitso ochuluka amene mudzasowe malo owayikamo.
Jehova Nyasaye Maratego wacho niya, “Keluru achiel kuom apar duto e od keno, mondo chiemo obed e oda. Tema uruane mondo une-ane ka donge dayawnu dirise mag dhorangeye polo mi aolnu gweth mogundho ma ok unyal yudo thuolo kama dukanie.
11 Ndidzaletsa tizirombo kuti tisawononge mbewu zanu, ndipo mpesa wa mʼminda mwanu zipatso zake sizidzayoyoka,” akutero Yehova Wamphamvuzonse.
Anagengʼ kute ma ok noketh chambu, kendo mzabibu manie puotheu olembgi ok notow mi lwar kapok ochiek,” Jehova Nyasaye Maratego owacho.
12 “Motero anthu amitundu yonse adzakutchulani odala, pakuti dziko lanu lidzakhala lokondweretsa,” akutero Yehova Wamphamvuzonse.
“Eka ogendini duto noluongu ni joma ogwedhi nikech pinyu nobed piny maber,” Jehova Nyasaye Maratego owacho.
13 Yehova akuti, “Mwayankhula mawu owawa onena za Ine. “Komabe inu mukufunsa kuti, ‘Kodi tanena chiyani chotsutsana nanu?’
Jehova Nyasaye wacho niya, “Usewuoyo marach kuoma. “To upenjo ni, ‘En angʼo ma wasewacho kuomi?’
14 “Mwanena kuti, ‘Kutumikira Mulungu nʼkosapindulitsa. Kodi timapindulanji pochita zofuna zake, ndi kumayenda ngati anamfedwa pamaso pa Yehova Wamphamvuzonse?
“Usewacho kama, ‘Tiyone Nyasaye onge tiende. En ohala mane ma wayudo kuom timo dwache kendo kuom wuotho ka waywagore e nyim Jehova Nyasaye Maratego?
15 Koma tsono ife timati anthu odzikuza ndiye odalitsika. Kunena zoona anthu oyipa ndiye amapeza bwino, ngakhale amene amanyoza Mulungu amapulumuka.’”
To waneno ni joma timbegi richo ema igwedho. Chutho joma timbegi richo dhi maber kendo kata gikwedo Nyasaye to gitony.’”
16 Ndipo woopa Yehova anayamba kukambirana, ndipo Yehova anamvetsera. Buku la chikumbutso linalembedwa pamaso pake, lonena za amene amaopa Yehova ndi kulemekeza dzina lake.
Eka joma ne oluoro Nyasaye nowuoyo e kindgi giwegi, kendo Jehova Nyasaye nochiko ite mowinjogi. Nying joma oluoro Jehova Nyasaye kendo mamiyo nyinge duongʼ nondiki e kitabu moro e nyime.
17 Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Anthu amenewo adzakhala anga, tsiku limene Ine ndidzachita izi, adzakhala angaanga. Ndidzawaleka osawalanga monga mmene munthu amachitira chifundo mwana wake amene amamutumikira.
Jehova Nyasaye Maratego wacho niya, “Ginibed joga, odiechiengʼno kendo anaketgi kaka mwanduna mageno. Anakechgi mana kaka ngʼato kecho wuode matiyone.
18 Pamenepo mudzaonanso kusiyana pakati pa anthu olungama ndi oyipa, pakati pa amene amatumikira Mulungu ndi amene satumikira Mulungu.”
Kendo unuchak une pogruok mane kind joma kare kod joma timbegi richo, kendo e kind joma tiyone Nyasaye gi joma ok tine.”

< Malaki 3 >