< Malaki 1 >

1 Uthenga: Mawu a Yehova kwa Israeli kudzera mwa Malaki.
Malakhi kut lamkah Israel ham BOEIPA olrhuh ol,
2 Yehova akuti, “Ine ndakukondani. Koma inu mukufunsa kuti, ‘Kodi mwatikonda motani?’” Yehova akuti, “Kodi Esau sanali mʼbale wake wa Yakobo? Komatu Ine ndinakonda Yakobo,
BOEIPA loh, “Nangmih kan lungnah,” a ti. Tedae, “Kaimih metlam nan lungnah? Esau tah Jakob manuca moenih a?” na ti uh. He tah BOEIPA kah olphong ni. Jakob he ka lungnah ngawn ta.
3 koma ndinamuda Esau, ndipo dziko lake lamapiri ndalisandutsa chipululu ndipo cholowa chake ndasiyira ankhandwe a mʼchipululu.”
Esau pataeng ka hmuhuet vaengah tah a tlang tlang te khopong la, a rho te khosoek pongui la ka poeh sak.
4 Mwina Edomu nʼkunena kuti, “Ngakhale taphwanyidwa, tidzamanganso mʼmabwinja.” Koma Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Iwo angathe kumanganso, koma Ine ndidzazigwetsanso. Iwo adzatchedwa dziko loyipa, la anthu amene Yehova wayipidwa nawo mpaka muyaya.
Edom loh, “N'laih coeng dae m'mael vetih imrhong khaw koep n'thoh bitni,” ti saeh. Caempuei BOEIPA loh he ni a thui. Amih loh thoh uh cakhaw ka koengloeng pah ni. Amih te halangnah khorhi la a khue uh vetih pilnam te BOEIPA loh kumhal duela kosi a hong thil ni.
5 Inu mudzaziona zimenezi ndi maso anu ndipo mudzati, ‘Yehova ndi Wamkulu, ukulu wake umafika ngakhale kunja kwa malire a Israeli!’
Na mik loh a hmuh vetih, “Israel khorhi voel duela BOEIPA len pai,” na ti uh ni.
6 “Mwana amalemekeza abambo ake, ndipo wantchito amaopa abwana ake. Ngati Ine ndine abambo anu, ulemu wanga uli kuti? Ngati ndine mbuye wanu, nanga kundiopa kuli kuti?” Akutero Yehova Wamphamvuzonse. “Ndinu, inu ansembe, amene mumanyoza dzina langa. “Komatu mukufunsa kuti, ‘Kodi timanyoza dzina lanu bwanji?’
Capa loh a napa, sal loh a boei a thangpom. Kai he pa la ka om atah kai thangpomnah tah melae? Kai boei atah kai taengah rhimomnah te melae? Caempuei BOEIPA he ni a thui. Nangmih khosoih loh ka ming na sawtsit lalah, “Na ming te metlam kan sawtsit?” na ti uh.
7 “Inu mwanyoza dzina langa popereka chakudya chodetsedwa pa guwa langa lansembe. “Komatu mukufunsa kuti, ‘Kodi ife takunyozani bwanji?’ “Mwandinyoza ponena kuti tebulo la Yehova ndi lonyozeka.
Ka hmueihtuk dongah aka mop loh buh a nok lalah, “Ba nen lae nang kan nok? Amah longni BOEIPA kah caboei a sawtsit,” na ti uh.
8 Mukamapereka nsembe nyama zosaona, kodi sicholakwa? Mukamapereka nsembe nyama zachilema kapena zodwala, kodi sicholakwa? Kayeseni kuzipereka kwa bwanamkubwa wanu! Kodi akasangalatsidwa nanu? Kodi akazilandira? Akutero Yehova Wamphamvuzonse.
Mikdael te nawn ham na mop uh vaengah a thae moenih a? Khokhaem neh aka ngoi na mop vaengah a thae moenih a? Na rhalboei taengah te te khuen uh mai lah, nangmih te m'moeithen aya? Na maelhmai te a dangrhoek aya? Caempuei BOEIPA loh he ni a thui.
9 “Tsopano tayesani kupempha Mulungu kuti akuchitireni chifundo. Kodi ndi zopereka zotere mʼmanja mwanu, Iye angakulandireni?” Akutero Yehova Wamphamvuzonse.
Te dongah Pathen mikhmuh ah kothae uh mai laeh. Te daengah ni mamih n'rhen eh. Nangmih kut lamkah aka thoeng nen he nangmih kah maelhmai te a doe aya? Caempuei BOEIPA loh he ni a thui.
10 “Ndikulakalaka mmodzi wa inu akanatseka zitseko za Nyumba ya Mulungu, kuti musayatsemo moto pachabe pa guwa langa lansembe! Ine sindikukondwera nanu,” akutero Yehova Wamphamvuzonse, “ndipo Ine sindidzalandira zopereka za mʼmanja mwanu.
Nangmih kongah unim thohkhaih aka khai lah ve. Te dongah ka hmueihtuk na sae sak uh pawh. Lunglilungla la, kai ham tah nangmih taengah ngaihnah tal coeng. Caempuei BOEIPA loh he ni a thui. Te dongah na kut lamkah khocang khaw ka doe mahpawh.
11 Dzina langa lidzalemekezedwa pakati pa mitundu ya anthu, kuchokera kummawa mpaka kumadzulo. Mʼmalo monse adzapereka nsembe zofukiza ndi zopereka zangwiro mʼdzina langa, chifukwa dzina langa lidzakhala lalikulu pakati pa mitundu ya anthu,” akutero Yehova Wamphamvuzonse.
Khomik kah khocuk lamloh a khuirhai duela namtom lakli ah ka ming len. Hlupnah hmuen takuem ah ka ming neh khocang cilh khaw na tawn uh. Namtom taengah ka ming he len pai tila Caempuei BOEIPA loh a thui.
12 “Koma inu mumalinyoza ponena kuti tebulo la Ambuye, ‘ndi lodetsedwa,’ ndipo chakudya chake, ‘nʼchonyozeka!’
Tedae, “Ka Boeipa kah caboei te amah loh a nok, a thaih neh a buh khaw a sit om,” na ti uh nen te na poeih uh.
13 Ndipo inu mumati, ‘Ndi zotopetsa zimenezi!’ Ndipo mumandinyogodola Ine,” akutero Yehova Wamphamvuzonse. “Pamene inu mubweretsa nyama zakuba, zolumala kapena zodwala ndi kupereka nsembe, kodi Ine ndizilandire kuchokera mʼmanja mwanu?” Akutero Yehova.
“Te te ngakyal la phen hmut te,” na ti uh. Caempuei BOEIPA loh a thui coeng. A huen phoeiah khokhaem neh aka ngoi ni na khuen tih khocang la na khuen uh. BOEIPA loh, “Nangmih kut lamkah te ka doe aya?” a ti.
14 “Atembereredwe munthu wachinyengo amene ali ndi nyama yayimuna yabwino mʼgulu la ziweto zake ndipo analumbira kuyipereka, koma mʼmalo mwake nʼkupereka nsembe kwa Ambuye nyama yosayenera. Yehova Wamphamvuzonse akuti, ‘Pakuti ndine mfumu yayikulu, dzina langa liyenera kuopedwa pakati pa anthu a mitundu yonse.’”
A tuping khuiah a tal a om lalah aka rhaithi hlang tah thae a phoei thil coeng. A caeng dae ka Boeipa ham tah a po a rhak ni a nawn. Caempuei BOEIPA loh, “Kai tah manghai puei la ka om tih ka ming he namtom taengah a rhimom,” a ti.

< Malaki 1 >