< Luka 8 >
1 Zitatha izi, Yesu anayendayenda kuchoka mzinda wina kupita wina ndiponso mudzi wina kupita wina, akulalikira Uthenga Wabwino wa ufumu wa Mulungu. Ophunzira ake khumi ndi awiri aja anali naye,
Gwejile gwalabhao mwanya mufuyi Yesu namba okugenda mumisi emitoto ne misi minene, nasimula no kulasha emisango jo bhwana jo bhukama bhwa Nyamuanga na bhaliya ekumi na bhabhili bhagendaga amwi nage.
2 komanso akazi ena amene anachiritsidwa ku mizimu yoyipa ndi matenda: Mariya, wotchedwa Magadalena, amene mwa iye munatuluka ziwanda zisanu ndi ziwiri;
kutyo kutyo bhagasi bhalebhe bhanu bhaliga bhaosibhwe okusoka ku masambwa amabhibhi na malwae gabhuli mbaga. Aliga ali Maliyamu unu atogwaga Magedalena unu aliga asosibhweko amasabwa saba.
3 Yohana mkazi wa Kuza, woyangʼanira mʼnyumba ya Herode; Suzana; ndi ena ambiri analinso. Akazi awa ankawathandiza ndi chuma chawo.
Yowana omugasi wa Kuza na omukulu wa Helode, Susana, na bhagasi abhandibhamfu, bhanu bhasosishe ebhinu bhyebhwe kwainjuno yebhwe abhene.
4 Anthu ambiri ankasonkhana, ndipo pamene anthu ankabwera kwa Yesu kuchokera ku midzi, Iye anawawuza fanizo ili,
Bhejile abhanu bhamfu bhakekumanya amwi, bhalimo na bhanu bhajaga kumwene okusoka mumisi jabhuli mbaga, alomele nabho kwebhijejekanyo.
5 “Mlimi anapita kukafesa mbewu zake. Akufesa mbewuzo, zina zinagwa mʼmbali mwa njira; zinapondedwa, ndipo mbalame zamlengalenga zinadya.
Omuyambi agendele okubhibha jimbibho, anu aliga nayamba, jimbibho ejindi nijigwa kumbali ya injila nijilibhatwa emwalo ya magulu, na jinyonyi ja mulutumba nijijilya.
6 Zina zinagwa pa thanthwe, ndipo pamene zinamera, zinafota chifukwa panalibe chinyezi.
Jimbibho ejindi nijigwa ingulu ya mayalu ganu gali kulutale na jejile jamela nijamba ofuka nijiotoka kulwokubha aliga gutalio munyililo.
7 Mbewu zina zinagwera pakati pa minga, zinakulira pamodzi ndi mingazo ndipo zinalepheretsa mmerawo kukula.
Jimbibho ejindi nijigwa mumati na mumawa, amati ago agamawa nigakula amwi na jimbibho ejo niga jinyiga.
8 Mbewu zina zinagwera pa nthaka yabwino. Zinamera ndipo zinabala mowirikiza 100 kuposa zimene zinafesedwa zija.” Atanena izi, anafuwula kuti, “Amene ali ndi makutu, amve.”
Nawe jimbibho ejindi jaguye mumayalu ga kisi nijibhula amatwasho kukila egana.”Yesu ejile amala okwaika amagambo ago, alomele kwo bhulaka bhunene naikati,”Wona wona unu ali na matwi no gwe.”
9 Ophunzira ake anamufunsa tanthauzo lake la fanizolo.
Lindi abheigisibhwa bhae nibhamubhusha ingulu ye chijejekanyo echo,
10 Iye anati, “Kudziwa zinsinsi za ufumu wa Mulungu kwapatsidwa kwa inu, koma kwa ena ndimawayankhula mʼmafanizo kuti, “ngakhale akuona, asapenye; ngakhale akumva, asazindikire.”
Yesu nabhabhila ati,”Muyanibhwe okumenya imbisike yo bhukama bhwa Nyamuanga, tali abhanu abhandi abheeigisibhwa ku lwebhijejekanyo ela, koleleki bhakalola bhatajakulola na bhakongwa bhatajakusombokelwa.'
11 “Tanthauzo la fanizoli ndi ili: Mbewu ndi mawu a Mulungu.
Na inu niyo insonga ye chijejekanyo chinu. Imbibhoni nigambo lya Nyamuanga.
12 Mbewu za mʼmbali mwa njira ndi anthu amene amamva mawu, ndipo kenaka mdierekezi amabwera ndi kuchotsa mawuwo mʼmitima mwawo kuti asakhulupirire ndi kupulumutsidwa.
Jimbibho jinu jaguye ayeyi na kunjila nibho bhanu bhanu abhongwa omusango, omusoko shetani nalisoshamo mumioyo jebhwe, koleleki bhasige okwikilisha nokuchungulwa.
13 Mbewu za pa thanthwe ndi anthu amene amalandira mawu mwachimwemwe pamene akumva, koma mawuwo sazika mizu. Iwo amakhulupirira kwa kanthawi, koma pa nthawi ya mayesero, amagwa.
Jinu jaguye kulutale ni bhanu bhanu abhongwa omusango nokugulamila kwo kusandabha nawe bhatali na misi jonajona, abhekilisha kwo mwanya mufuyi, no mwanya gwokulegejibhwa nibhagwa.
14 Mbewu zimene zinagwa pakati pa minga zikuyimira anthu amene amamva mawu, koma akamayenda mʼnjira zawo amatsamwitsidwa ndi zodandaulitsa za moyo uno, chuma ndi zosangalatsa, ndipo iwo samakhwima.
Na jimbibho jinu jaguye mumawa ni bhanu bhanu abhongwa omusango, nawe bhakagendelela okukula nibhaingililwa nokufulubhendela obhunibhi no bhukonde bhwo bhulame na bhatakwibhula matwasho.
15 Koma mbewu za pa nthaka yabwino zikuyimira anthu amene ali ndi mtima woona ndi wabwino, amene amamva mawu nawasunga, ndipo amalimbikira mpaka amabala zipatso.
Nawe jimbibho jinu jaguye mumayalu gakisi nibhanu bhanu, bhali nobhikeyi ne mioyo jakisi, bhakongwa omusango abhaligwatilila na abhebhula amatwasho go kwikomesha.
16 “Palibe amayatsa nyale ndi kuyibisa mu mtsuko kapena kuyika pansi pa bedi. Koma mʼmalo mwake, amayika pa choyikapo chake, kuti anthu olowamo aone kuwala.
Woli anu, atalio nolo umwi, unu kakongesha itala naifundikila naimbakuli au naita mubhutalaasi. Nalema okuita kungango koleleki bhuli unu kengila abhone okuilola.
17 Pakuti palibe kanthu kobisika kamene sikadzawululika, ndipo palibe kanthu kophimbika kamene sikadzadziwika kapena kuonetsedwa poyera.
Kulwokubha chitalio chinu chiliseleka nichilema okumenyekana, au chonachona chinu chili cha mumbisike chinu chitali bhonekana kubwelu.
18 Choncho ganizirani mozama. Iye amene ali nazo adzapatsidwa zambiri, iye amene alibe, ngakhale chimene akuganiza kuti ali nacho adzalandidwa.”
Kulwejo nubhe mwengeso anu ulabhaga nutegelesha. Kulwokubha unu ali nacho, kongesibhwa lindi, nawe unu atanacho nolo kanu alinako akatilu kona akagegibhwa.”
19 Tsopano amayi ndi abale a Yesu anabwera kudzamuona Iye, koma analephera kuti afike pafupi ndi Iye chifukwa cha gulu la anthu.
Eile nyilamwene Yesu na bhamula bhabho nibhaja kumwene bhatamulebhelee kulwokubha lyaliga lilio eijo enene lya bhanu.
20 Wina anamuwuza Iye kuti, “Amayi ndi abale anu ayima kunja, akufuna kukuonani.”
Nibhamubhwila,”Nyokomwana na bhamula bhanyu bhalianja abhakwenda.
21 Yesu anayankha kuti, “Amayi ndi abale anga ndi amene amamva mawu a Mulungu ndi kumachita zimene mawuwo akunena.”
Nawe Yesu, nabhasubhya naikati,”Mayi wani na bhamula bhasu ni bhanu abhongwa omusango gwa Nyamuanga no kugwimako.”
22 Tsiku lina Yesu anati kwa ophunzira ake, “Tiyeni tiwolokere tsidya lina la nyanja.” Ndipo analowa mʼbwato nanyamuka.
Munaku ejo Yesu na bheigisibhwa bhae nibhalinya mubhwato, nabhabhwila ati, “Chambuke chigende ku ngego ya kabhili yo mwalo.” Nibhachumachuma obhwato bhwebhwe.
23 Akuwoloka, Iye anagona tulo. Namondwe wamkulu anayamba pa nyanja, ndipo bwatolo linayamba kudzaza ndi madzi ndipo anali pa chiopsezo chachikulu.
Nawe bhejile bhamba okwimuka, Yesu namama naongela, nomuyaga mwamfu ogwe chiule, obhwato bhwebhwe nibhwijula amanji bhaliga bhali munyanko nene muno.
24 Ophunzira anapita ndi kukamudzutsa Iye, nati, “Ambuye, Ambuye, ife tikumira!” Anadzuka ndipo anadzudzula mphepo ndi madzi owindukawo. Namondwe anasiya, ndipo panali bata.
Bheile abheigisibhwa bhae nibhamwimusha, nibhaikati,”Latabhugenyi mkulu! Latabhugenyi mkulu! chiliayeyi okufwa!”Nemuka nagonya omuyaga na makonjo ga manji nigafungama na ndibha etole.
25 Iye anafunsa ophunzira ake kuti, “Chikhulupiriro chanu chili kuti?” Koma pogwidwa ndi mantha ndi kudabwa anafunsana wina ndi mnzake kuti, “Uyu ndi ndani? Iye alamulira ngakhale mphepo ndi madzi, ndipo zimumvera Iye.”
Lindi nabhabhwila ati,”Elikilisha lyemwe liliaki?”Nibhobhaya, Nibhatanga'ngala, nibhaikana bhuli munu no wejabho,”Unu niga, unu kagonya omuyaga na manji nigafung'ama?”
26 Iwo anawolokera ku chigawo cha Gerasa chimene chili tsidya lina la nyanja kuchokera ku Galileya.
Nibhakinga mumusi gwa Gelasini inu ili inyuma yo musi gwa Galilaya.
27 Yesu ataponda pa mtunda, anakumana ndi munthu wogwidwa ndi ziwanda wochokera mu mzindawo. Kwa nthawi yayitali munthuyu sanavale zovala kapena kukhala mʼnyumba, koma amakhala ku manda.
Yesu ejile atuka nataja kuchalo, omunu umwi okusoka mujini, nabhugangana nage, no munu unu aliga ali na masabhwa. kwo mwanya mulela aliga atakufwala ngubho, na aliga atakwikala munyumba, tali aliga nekala enu bhasikaga abhafuye.
28 Iye ataona Yesu, anakuwa nagwa pa mapazi ake akufuwula kwambiri kuti, “Mukufuna chiyani ndi ine, Yesu Mwana wa Mulungu Wammwambamwamba? Ndikupemphani Inu, musandizunze ine!”
Ejile amulola Yesu nalila kwo bhulaka, nagwa ansi imbele yae. kwo bhulaka bhunene naikati, Nakoleleki anye kwawe, Yesu omwana wa Nyamuanga unu ali ingulu? Enikulembeleja, utaja kunyasha anye”
29 Pakuti Yesu analamula mzimu woyipawo kuti utuluke mwa munthuyo. Kawirikawiri umamugwira iye, ndipo ngakhale anali womangidwa ndi unyolo dzanja ndi mwendo ndi kuti ankamuyangʼanira, koma amadula maunyolo akewo ndipo ziwanda zimamutengera kumalo a yekha.
Yesu nalagilila amasabwa ago amabhibhi gamusokeko omunu oyo, kulwokubha mwanya mwamfu aliga asalile. Nolwo kutyo aliga abhoelwe ne minyololo no kutulwa ansi yo bhangalisi, abhutulaga nokulibhasibhwa okukinga mwibhala.
30 Yesu anamufunsa kuti, “Dzina lako ndani?” Iye anayankha kuti, “Legiyo,” chifukwa ziwanda zambiri zinalowa mwa iye.
Yesu namubhusha ati,”Lisina lyao nawega?”nasubhya naikati, “Legioni”Kulwokubha amasabwa mamfu gengiye kumwene.
31 Ndipo ziwandazo zimamupempha mobwerezabwereza kuti asazitumize ku dzenje la mdima. (Abyssos )
Njigendelela okumulembeleja utachilagilila okuja mulyobho. (Abyssos )
32 Gulu lalikulu la nkhumba limadya pamenepo mʼmbali mwa phiri. Ziwandazo zinamupempha Yesu kuti azilole kuti zikalowe mu nkhumbazo ndipo Iye anazilola.
Liijo lya jingulubhe lyaliga ndilebhwa ingulu ya libhanga, nibhamulembeleja abhabhile bhengile mu ngulubhe. Nabhekilisisha bhakole kutyo.
33 Ziwanda zija zitatuluka mwa munthuyo, zinakalowa mwa nkhumbazo, ndipo gulu lonselo linathamangira ku mtsetse ndi kukalowa mʼnyanja ndi kumira.
Kulwejo amasabwa ago nigamusokako omunu oyo nigengila mungulubhe, na liijo nilibhilimila kuchima nibhagwilila mumanji nibhafwila omwo.
34 Oweta nkhumbazo ataona zimene zinachitikazo, anathamanga ndi kukanena izi mu mzinda ndi ku madera a ku midzi.
Abhanu bhanu bhaliga nibhalebha jingulubhe ejo bhejile bhalola chinu chabhao, nibhabhilima na nibhajaokwaika mumusi na mumisi jinu jaliga jibheindileko.
35 Ndipo anthu anapita kukaona zimene zinachitika. Atafika kwa Yesu, anapeza munthu amene anatulutsidwa ziwanda uja atakhala pa mapazi a Yesu, atavala ndipo ali ndi nzeru zake; ndipo iwo anachita mantha.
Abhanu bhejile bhakongwa ago nibhaja okulola jinu jabhonekana, na nibhaja ku Yesu nibhamulola omunu amasabhwa galiga gamusokeleko. aliga afwae kisi na ali no bhwenge bhwa kisi, enyanjile kumagulu ga Yesu, nibhobhaya.
36 Amene anaona izi anawuza anthu mmene munthu wogwidwa ndi ziwandayo anachiritsidwira.
Niwo oumwi webhwe unu alolele chinu chabhonekene namba okubhabhwila abhandi kutyo omunu oyo unu aliga natangasibhwa na masabhwa kutyo eulisibhwa.
37 Kenaka anthu onse a ku chigawo cha Gerasa anamupempha Yesu kuti achoke kwa iwo, chifukwa anadzazidwa ndi mantha. Choncho Iye analowa mʼbwato nachoka.
Abhanu bhona abhomukowa gwa Wagelasi na bhanu bhaliga bhasijene nibhamusabhwa Yesu abhasokeko kulwokubha bhaliga bhali no bhubha bhamfu. Nengila mubhwato nasubhayo.
38 Munthu amene anatulutsidwa ziwanda uja, anapempha Yesu kuti apite nawo, koma Yesu anamubweza nati,
Omunu unu asosibhweko emisabhwa namulembeleja Yesu agende nage, nawe Yesu namubhwila agende no kwaikati,
39 “Bwerera kwanu kafotokoze zimene Mulungu wakuchitira.” Ndipo munthuyo anachoka ndi kukanena ku mzinda wonsewo zimene Yesu anamuchitira iye.
“Subha mumusi gwao na ubhale gona ganu Nyamuanga akukolela”. Omunu oyo nagenda, nalasha mumusi gwona ganu Yesu amukolela omwene,
40 Yesu atabwerera, gulu lalikulu la anthu linamulandira, chifukwa onse ankamuyembekezera.
Yesu nasubha, abhanu bhamfu nibhamulamila, kulwokubha bhona bhaliga bhamutegelee.
41 Nthawi yomweyo munthu wotchedwa Yairo, woweruza wa mu sunagoge, anabwera ndi kugwa pa mapazi a Yesu, namupempha Iye kuti apite ku nyumba kwake,
Lola naja munu umwi unu atogwaga Yailo ni umwi wa bhatangasha mulikofyanyisho. Yailo nagwa mumagulu ga Yesu namwilembeleja agende ika ewae.
42 chifukwa mwana wake yekhayo wamkazi, kamtsikana ka zaka khumi ndi ziwiri, kanali pafupi kufa. Pamene Yesu ankapita gulu la anthu linkamupanikiza.
Kulwokubha aliga ali no mwana muyala umwila, unu aliga ali ne miyaka kumi ne bhili, ali mumwanya gwo kufwa. Anu aliga nagenda, bhanu bhamfu nibhamuiganya omwene.
43 Ndipo pomwepo panali mayi wina amene ankataya magazi kwa zaka khumi ndi ziwiri, koma panalibe wina akanamuchiritsa.
Omugasi unu aululaga insagama kwe miyaka ekumi ne bhili aliga alio awo amalile jiela jae kubhafumu, nawe atalio na umwi unu aliga amuosishe.
44 Iye anafika kumbuyo kwake ndi kukhudza mothera mwa chovala chake, ndipo nthawi yomweyo magazi ake analeka kutuluka.
Naja inyuma ya Yesu nakunyako kwipindo lyo mwenda gwae, aonao okusoka insagama kwae nikutemekela.
45 Yesu anafunsa kuti, “Wandikhudza ndani?” Onse atakana, Petro anati, “Anthu akukupanikizani ndi kukukankhani.”
Yesu naikati, Niga unu ankunyako?”Bhejile bhalema bhona, Petelo naikati, Latabhugenyi, abhanu ni bhamfu munu bhanu abhakukula no kukuiganya.”
46 Koma Yesu anati, “Wina wandikhudza; ndikudziwa chifukwa mphamvu yachoka mwa Ine.”
Nawe Yesu naikati,”Omunu umwi ankunyako, okubha namenya amanaga gansokamo.”
47 Ndipo mayiyo podziwa kuti sanathe kuchoka wosadziwika, anabwera akunjenjemera ndipo anagwa pa mapazi a Yesu. Pamaso pa anthu onse, anafotokoza chifukwa chimene anamukhudzira Iye ndi mmene iye anachiritsidwira nthawi yomweyo.
Omugasi ejile alolati atakutula kuseleka chinu akola, namba okuyalala, nagwa ansi imbele ya Yesu nabhwila abhanu bhona chinu chakola amukunyeko na kutyo eulisibhwa aonao.
48 Kenaka anati kwa iye, “Mwana wamkazi, chikhulupiriro chako chakuchiritsa. Pita mu mtendere.”
Neya naika nage ati,”Muyala, elikilisha lyao lyakola ubhe muanga. Genda no mulembe.”
49 Pamene Yesu ankayankhulabe, munthu wina anabwera kuchokera ku nyumba ya Yairo, woweruza wa ku sunagoge uja. Iye anati, “Mwana wanu wa mkazi wamwalira, musawavutitsenso Aphunzitsiwa.”
Mbe anu aliga achaika, omunu umwi naja okusoka munyumba yo mutangasha we likofyanyisho, naikati,”Omuyansha wao afuye. Siga okumunyasha omwiigisha.”
50 Atamva zimenezi, Yesu anati kwa Yairo, “Usachite mantha, ingokhulupirira basi ndipo adzachiritsidwa.”
Nawe Yesu ejile ongwa kutyo, namusubhya naikati,”Utaja kubhaya. Ikilishala, nakakila.”
51 Iye atafika ku nyumba ya Yairo, sanalole wina aliyense kulowa kupatula Petro, Yohane, ndi Yakobo ndi abambo ndi amayi a mwanayo.
Mbe bhejile bhengila munyumba eyo, atekilisishe munu undi okwingila nage, tali Petelo, Yowana na Yakobho, esemwene omwana na nyila mwene.
52 Pa nthawiyi nʼkuti anthu onse akubuma ndi kumulirira iye. Yesu anati, “Lekani kulira, sanafe koma wagona tulo.”
Ao abhanu bhona bhaliga nibhalila kwo bhulaka, nawe naikati,”Musige okusekana, achali kufwa, nawe amamilela.”.
53 Iwo anamuseka podziwa kuti anali atamwalira.
Nawe nibhamuseka kwo kumugaya, okubha bhaliga bhamenyele ati afuye.
54 Koma Iye anamugwira dzanja lake ndipo anati, “Mwana wanga, dzuka!”
Nawe omwene, namugwata omuyala okubhoko, nabhilikila kwo bhulaka, naika ati,”Mwana imuka”
55 Mzimu wake unabwerera, ndipo nthawi yomweyo anayimirira. Kenaka Yesu anawawuza kuti amupatse chakudya.
Omwoyo gwae nigusubhamo, nemuka omwanya ogwo ogwo, Nabhalagilila ati, ayabhwe echinu cho kulya abhone okulya.
56 Makolo ake anadabwa, koma Iye anawalamulira kuti asawuze wina aliyense zimene zinachitikazo.
Abhebhusi bhae nibhalugula, nawe nabhabhwila bhasiga kubhwila munu kutyo jabha.