< Luka 5 >

1 Tsiku lina Yesu anayima mʼmbali mwa nyanja ya Genesareti, gulu la anthu litamuzungulira likumvetsera mawu a Mulungu.
Ik aaw Iyesus Genseret' aats k'ari gúratse need' dek't b́ befere ay ashuwots b́ maants t'int Ik'i aap'tso k'ebosh bo gifniyefere bo teshi.
2 Iye anaona mabwato awiri ali mʼmphepete mwa nyanja, asodzi amene ankachapa makhoka awo atawasiya pamenepo.
Bí aats k'ari gúrats t'iindek't need'iru jelb gitwotsi bek'b́k'ri, mus' detsirwotsmó jelbwotsitse kesht bo mus'i kambwotsi bo mashfera botesh.
3 Iye analowa mʼbwato limodzi limene linali la Simoni, ndi kumupempha kuti alikankhire mʼkati mwa nyanja pangʼono. Kenaka Iye anakhala pansi nayamba kuphunzitsa anthu ali mʼbwatomo.
Iyesus jelbwotsitsi iku, Simoonk wottsuts b́ kindi. Simonshowere «Jelbani datsatse aats k'aromaants aab taash t'intswe» bí et. Maniye okoon jelbú'ats bedek't ash asho b́ daniyiri b́ tesh.
4 Atatha kuyankhula anati kwa Simoni, “Kankhirani kwa kuya ndipo muponye makhoka kuti mugwire nsomba.”
B́ keewrwo b́ ishyakon Sim'onsh, «Jelbu ay dek't k'arts aats k'aromaants wokide'er neenat n tohuwotsn mus' detsosh juwore, » b́ et.
5 Simoni anayankha kuti, “Ambuye, tagwira ntchito molimbika usiku wonse, koma sitinagwire kanthu. Koma pakuti mwatero, ndiponya makhoka.”
Sim'onwere «Danifono! t'ú jamo maawron gatsaat eegor deshatsone, nee ni'etihakonmó, hambe! mus'i kambo shap'etwone, » bí et.
6 Atachita izi, anagwira nsomba zambiri kotero kuti makhoka awo anayamba kungʼambika.
Mus'i kambman bo shap'tsok'on kambo b́ gad'efetso weeralo ayts mus'o detsbodek'i.
7 Choncho anakodola anzawo a bwato linalo kuti abwere ndi kuwathandiza, ndipo anabwera nadzaza mabwato onse awiri mpaka kuyamba kumira.
Mansh k'osh jelbutse fa'a bo tohuwotsi kolon waar boosh geetso bo dabitwok'o bo s'eeǵ, boowere waat git jelbuwots limosh muk'i boborfetsosh mus'on s'eents bok'r.
8 Simoni Petro ataona izi, anagwa pa mawondo a Yesu nati, “Chokani kwa ine Ambuye: Ine ndine munthu wochimwa!”
Simon P'et'ros man bek'b́k'rtsok'on Iyesus shinats tuk'umalgutsat, «Doonzono, Taa morretsk t wottsotse t maants t'ink'aye!» bí et.
9 Iye ndi anzake onse anadabwa ndi nsomba zimene anagwira,
Han bíettsonwere bínat bínton teshts b́ tohjamwots bo detsts mus'i aytsatse tuutson ayidek't adt boteshtsotsna.
10 chimodzimodzinso Yakobo ndi Yohane, ana a Zebedayo, anzake a Simoniyo. Kenaka Yesu anati kwa Simoni, “Musachite mantha; kuyambira tsopano ndidzakusandutsani asodzi a anthu.”
Mank'o Sim'on tooh wottswots Zebdiwos nanawots Yak'obnat Yohansń adtni botesh. Iyesus Simonsh «Shenono shatk'aye, Haniyehakon ash detsetwo wotitune» bí et.
11 Kenaka anakokera mabwato awo ku mtunda, nasiya zonse namutsata Iye.
Bowere jelbuwotsi aats gúúrats bot'intsi hakon jam keewo k'azk'rat Iyesus shuuts shoydek't botuwi.
12 Yesu ali ku mudzi wina, munthu amene anali ndi khate thupi lonse anabwera kwa Iye. Munthuyo ataona Yesu, anagwa chafufumimba ndipo anamupempha Iye kuti, “Ambuye, ngati mukufuna, mukhoza kundiyeretsa.”
Ik aaw Iyesus kit ikutse b́befere bíatso een shodon detsetso, eenshodonwere bí ats jamats keshutstso ash iko b́ maants b́ waa, Iyesusi b́ bek'ktsok'on b́ baron datsats gúp'gup'dek't t doonzo «Ni eekiyal taan s'ayintso falfne, » et bín b́ k'oni.
13 Yesu anatambasula dzanja lake namukhudza munthuyo. Iye anati, “Ine ndikufuna, yeretsedwa!” Ndipo nthawi yomweyo khate lake linachoka.
Iyesuswere b́ kisho jargdek' bín shuu'at «Eekere! s'ayine!» bí et. Ashmanwere manoor b́ een shodatse s'ayin b́wutsi.
14 Kenaka Yesu anamulamula kuti, “Usawuze wina aliyense, koma pita, kadzionetse kwa wansembe ndi kukapereka nsembe zimene Mose anakulamulirani za kuyeretsedwa kwanu monga umboni kwa iwo.”
Manats dabt hank'o ett bí azazi «Keewan konshor nkewrawok'owa, ernmó niamtsok'on n tooko kahniwotssh kitswe, ash jamosh gaw b́wotitwok'owa n s'ayintsi jango Muse b́ azaztso woshoono t'intswe.»
15 Koma mbiri yake inafalikirabe kwambiri kotero kuti magulu a anthu anabwera kudzamvetsera ndi kuti achiritsidwe ku matenda awo.
Iyesus shútso iki k'oshortsoniyere bogo shiye b́guuts, ay ashuwotswere b́keewo k'ebonat boshodotse kashosh geeyat bo kakuwefo.
16 Koma Yesu nthawi zambiri ankachoka kupita ku malo a yekha kukapemphera.
Bímó ash aalok k'ayamrni Ik'o b́ k'onfo.
17 Tsiku lina pamene ankaphunzitsa, Afarisi ndi aphunzitsi amalamulo, amene anachokera ku midzi yonse ya Galileya ndi ku Yudeya ndi Yerusalemu, anakhala pansi pomwepo. Ndipo mphamvu ya Ambuye inalipo yakuti Iye achiritse odwala.
Ik aaw Iyesus daniyoke b́befere ferisawi eteetswotsnat Muse nemo danifwotsn b́ganoke bedek'tni bo tesh, bo Gelilnat Yihud gál jamotse Iyerusalem kitotsnowere watswotsu fa'ano botesh. Iyesus shodetswotsi b́ kashiru doonzo ango bíntoni b́tesh.
18 Amuna ena anabwera atanyamula munthu wofa ziwalo pa mphasa ndipo anayesa kumulowetsa mʼnyumba kuti amugoneke pamaso pa Yesu.
Ash dúr iko es'oń kur dek'ts ash ashuwots Iyesusmaants dek't bowaa, Iyesus bítse b́ beyiru moots kindsh de'er b́shinats beezo geyatni bo tesh,
19 Atalephera kupeza njira yochitira zimenezi chifukwa cha gulu la anthu, anakwera naye pa denga ali pa mphasa pomwepo ndi kumutsitsira mʼkati pakati pa gulu la anthu, patsogolo penipeni pa Yesu.
Ernmó asho bí'aytsatse tuutson durman moots kindsho bomaaw, mansh máá tookats dek' bokesh, máá tokono wogdek't máá maac'ots bí'es'onton Iyesus shinats orshdek't gedebok'ri.
20 Yesu ataona chikhulupiriro chawo, anati, “Mnzanga, machimo ako akhululukidwa.”
Iyesuswere bo aman amano b́bek'tsok'on durosh, «Ashono neena! n morro niatse sholbazere, » bí et.
21 Afarisi ndi aphunzitsi amalamulo anayamba kuganiza mwa iwo okha kuti, “Kodi munthu uyu ndi ndani amene ayankhula zamwano? Kodi ndani amene angakhululukire machimo kupatula Mulungu?”
Nem danifuwotsnat ferisawino etefwotsn «Kone bíwo Ik'o c'ashirwani? Ash morro oorowe etosh falitwo Ik'oniye okoon k'osho kone fa'oni?» ett bo gitsotse bo gawfera botesh.
22 Yesu anadziwa zomwe iwo amaganiza ndipo anafunsa kuti, “Kodi ndi chifukwa chiyani mukuganiza zimenezi mʼmitima mwanu?
Iyesuswere bo bogawirman dank'rat boosh hank'o bíet, «It nibotse eegoshe hank'o it gawiri?
23 Kodi chapafupi ndi chiti: kunena kuti, ‘Machimo ako akhululukidwa,’ kapena kunena kuti, ‘Nyamuka ndipo yenda?’”
B́woteferemó ‹N morro neesh oorowe› etonat, ‹Tuur amee!› etotse aaw ketefa?
24 Koma kuti inu mudziwe kuti Mwana wa Munthu ali ndi ulamuliro pa dziko lapansi wokhululukira machimo, Iye anati kwa munthu wofa ziwaloyo, “Ine ndikuwuza iwe kuti, ‘Imirira, nyamula mphasa ndipo uzipita kwanu.’”
Ernmó ash na'o datsatse morro oorowe etosh alo b́detstsok'o dano itsh geyife» ett ash durmansh, «Ashono neena tuuwe, ni es'o kur de'er n galomand amee!» bí eti.
25 Nthawi yomweyo anayimirira patsogolo pawo, nanyamula mphasa yake ndipo anapita kwawo akuyamika Mulungu.
Dúronwere manoor ash ashuwots shinatse tuut, bíats k'eedek't b́teshts es'o kurdek't, Ik'o údefere b́ galomand bí ami.
26 Aliyense anadabwa ndi kuchita mantha ndipo anayamika Mulungu. Iwo anadabwa kwambiri ndipo anati, “Lero taona zinthu zosayiwalika.”
Manoke fa'a ash jamwotswere ayidek't adfetst, shatoon «Hambets adits keewo bek'rone, » etfetst Ik'o bo údi.
27 Zitatha izi, Yesu anachoka ndipo anaona wolandira msonkho dzina lake Levi atakhala mʼnyumba ya msonkho. Yesu anati kwa iye, “Nditsate Ine.”
Maniyere il Iyesus manoke kesht bíamfere Lewi eteetso t'ilish ko'ifo t'ilish b́dek'foke b́befere bek'krat «T shuutso wowe» bí et.
28 Ndipo Levi anayimirira, nasiya zonse ndi kumutsata Iye.
Lewi were jobk' ett jamó k'azk'rat b́ shuutso bíami.
29 Kenaka Levi anakonzera Yesu phwando lalikulu ku nyumba yake ndipo gulu lalikulu la amisonkho ndi ena ankadya naye pamodzi.
Maniye il Lewi b́mootse Iyesus mangosha ett een wotts móónat úshon k'aniyi b́k'ri, b́ k'anits móónat úshono t'ilish kakuf ayuwotsnat k'oshwotsu ay ash ashuwotsu datseyatni botesh.
30 Koma Afarisi ndi aphunzitsi amalamulo amene anali a gulu lawo anadandaula kwa ophunzira ake, “Kodi ndi chifukwa chiyani mukudya ndi kumwa pamodzi ndi amisonkho ndi ochimwa?”
Ferisawi eteefwotsnat bo jir wotts nem danifwots «T'ilish ko'ifwotsntonat morrotswotsnton maat b́ úshiri eegoshe?» ett Iyesus danifuwots aats bo mumund.
31 Yesu anawayankha kuti, “Amene sakudwala safuna singʼanga, koma odwala.
Iyesus hank'o et boosh bí'anyi, «Shodtswotssha bako jeenwotssh atetso geyiratse,
32 Ine sindinabwere kudzayitana olungama, koma ochimwa kuti atembenuke mtima.”
Taa t wáá morretswots naandrone bo etetwok'o s'eegosha bako kááwwotsi s'egoshaliye.»
33 Iwo anati kwa Iye, “Ophunzira a Yohane amasala kudya ndi kupemphera kawirikawiri, monganso ophunzira a Afarisi, koma anu amangodya ndi kumwa.”
Ik ik ashuwots Iyesussh, «Yohansnat ferisawiwotsn bo danifwots ayoto s'oomefno, Ik'ono k'onfnere, n danifwots jam aawo máát bo'úshir eegoshe?» ett bín boaati.
34 Yesu anawayankha kuti, “Kodi alendo a mkwati angasale kudya pamene mkwati ali pakati pawo?
Iyesuswere hank'o ett boosh bí aani, «Guuyo bonton b́befere guuy jishfwots bo s'oomo boosh geyitwe etatnya it gawiri?
35 Koma nthawi ikubwera pamene mkwati adzachotsedwa pakati pawo. Masiku amenewo adzasala kudya.”
Ernmó guuyo booke k'a'údek'et aawo weetwe, manoor s'oomitúne.»
36 Iye anawawuza fanizo ili: “Palibe amene amangʼamba chigamba kuchokera pa chovala chatsopano ndi kuchisokerera pa chakale. Ngati atatero, ndiye kuti adzangʼamba chovala chatsopanocho, ndipo chigamba chochokera pa chovala chatsopano chija sichidzagwirizana ndi chakale.
Manatse tuut Iyesus jewrdek' boosh ik keewo b́keewi, «Shemi handri but'o shemi nataats shipfo konwor aaliye, mank'o b́k'aliyalmó shemi handro gad'ni b́k'riti, but'i handronwere shemi natosh woteratse.
37 Ndipo palibe amene amakhuthulira vinyo watsopano mʼmatumba a vinyo akale. Ngati atatero, vinyo watsopanoyo adzaphulitsa zikopazo, vinyo adzatayika ndipo zikopa za vinyozo zidzawonongeka.
Mank'o weyni biri arwi natots weyni biri handro gas'fo aaliye, gas'eyalmó weyni biri handrman aruman t'up'inibk'riti, weyni birmanwere kud'ni b́gutsiti, arwonwere finats jinatse.
38 Ayi, vinyo watsopano ayenera kuthiridwa mʼmatumba a vinyo azikopa zatsopano.
Mansh weyni handr biro arwi handrots gaas'o geyife,
39 Ndipo palibe amene atamwa vinyo wakale amafuna watsopano, pakuti amati, ‘Wakale ndi okoma.’”
Weyni biri kats úshtso weyni biri beno úsho geeratse, ‹Ja'atso weyni biri katso k'anefe, › bí eteti.»

< Luka 5 >