< Luka 4 >
1 Yesu, wodzazidwa ndi Mzimu Woyera, anachoka ku mtsinje wa Yorodani ndipo anatsogozedwa ndi Mzimu Woyerayo kupita ku chipululu,
Neya, Yesu ejuye Omwoyo Mwelu, nasubha okusoka mumugela gwa Yelodani, atangasibhwe no Mwoyo okuja mwibhala.
2 kumene anayesedwa ndi mdierekezi masiku makumi anayi. Sanadye kena kalikonse pa masiku amenewo, ndipo pa mapeto pake anamva njala.
Kwa nsiku makumi gana, neyo nalegejibhwa na shetani. Omwanya ogwo atalyaga chinu chonachona, no bhutelo onguhye injala.
3 Mdierekezi anati kwa Iye, “Ngati ndiwe Mwana wa Mulungu, uza mwala uwu kuti usanduke buledi.”
Shetani namubhwila ati,”Labha uli mwana wa Nyamuanga, libhwile libhuyi linu gubhe mukate.”
4 Yesu anayankha kuti, “Zalembedwa: ‘Munthu sadzakhala ndi moyo ndi chakudya chokha.’”
Yesu nasubhya naikati,”Jandikilwe, omunu atakulama kwe mikate jenyele.”
5 Mdierekezi anamutengera Iye pamalo aatali ndipo mʼkamphindi namuonetsa maufumu onse a dziko lapansi.
Neya Shetani namutangasha okuja kuchinsonge che chima, namwolesha obhuka bhwona bhwe chalo kwo mwanya mufuyi.
6 Ndipo anati kwa Iye, “Ndidzakupatsani ulamuliro ndi ulemerero wawo; pakuti anandipatsa ine, ndipo ndingathe kupereka kwa aliyense amene ndikufuna.
Shetani namubhwilati,”Enikuyana obhutulo obhwokukama amwi na likusho lyabho. Enitula okukola kutyo kulwokubha niyanibhwe bhyona nibhikame, na enitula okumuyana wonawona unu enenda.
7 Ngati mutandilambira, zonsezi zidzakhala zanu.”
Kulwejo, ukanyifukamila no kundamya, ebhinu bhyona bhinu ebhibha bhyawo.”
8 Yesu anayankha kuti, “Zalembedwa: ‘Pembedza Yehova Mulungu wako ndi kumutumikira Iye yekha.’”
Tali Yesu asubhishe namubhwilati,”Yandikilwe, Nibhusibhusi umulamye Latabhugenyi Nyamuanga wao, na nibhusibhusi umukolele omwene ela.”
9 Mdierekezi anapita naye ku Yerusalemu namuyimiritsa pamwamba penipeni pa Nyumba ya Mulungu. Ndipo anati, “Ngati ndinu Mwana wa Mulungu dziponyeni nokha pansi kuchokera pano.
Amalile Shetani namutangasha Yesu okukinga Yelusalemu namuta ingulu chimwi eya liyekalu namubhwilati,”Labha uli mwana wa Nyamuanga nulagale ansi okusokanu.
10 Pakuti kwalembedwa, “Adzalamulira angelo ake za iwe kuti akutchinjirize mosamala;
Kulwokubha yandikilwe,”Kabhalagilila bha malaika bhae bhakulamile no kukulinda,
11 ndipo adzakunyamula ndi manja awo, kuti phazi lako lisagunde pa mwala.”
na abhakwimusha ingulu mumabhoko gebhwe koleleki utaja kuutasha amagulu gao ingulu ya mabhuyi”
12 Yesu anayankha kuti, “Mawu akuti, ‘Musamuyese Yehova Mulungu wanu.’”
Yesu nasubhya namubhwilati, “Jaiikilwe,”utamulegeja Latabhugenyi Nyamuanga wao.”
13 Mdierekezi atamaliza mayesero awa onse, anamusiya Iye kufikira atapeza mpata wina.
Shetani ejile amala okumulegeja Yesu, nagenda jae namusiga kukinga mwanya gundi.
14 Yesu anabwerera ku Galileya mu mphamvu ya Mzimu Woyera, ndipo mbiri yake inafalikira ku madera onse a ku midzi.
Neya Yesu nasubha Galilaya kwa managa go Mwoyo, na jinkuma jae nijiswila muchalo chona chinu aliga bhasijene nacho chona.
15 Iye ankaphunzitsa mʼmasunagoge awo, ndipo aliyense ankamulemekeza.
Eiigisishe mu mekofyanyisho gebhwe, na bhuli munu amukuyishe
16 Iye anapita ku Nazareti, kumene anakulira, ndipo pa tsiku la Sabata anakalowa mʼsunagoge, monga mwa chikhalidwe chake. Ndipo anayimirira kuti awerenge malemba.
Lusiku lumwi agendele Najaleti, omusi gunu ebhuliwemo nokukulilamo. Lwakutyo yaliga ili ntugwa yae nengila mulikofyanyisho olusiku lwa isabhato, emeleguyu no kusoma amaandiko.
17 Anamupatsa buku la mneneri Yesaya. Atalitsekula, anapeza pamalo pamene panalembedwa kuti,
Ayanibhwe echitabho cho mulagi Isaya, kulwejo, nafumbula echitabho naiga anu kandikilwe,
18 “Mzimu wa Ambuye ali pa Ine; chifukwa wandidzoza kuti ndilalikire Uthenga Wabwino kwa osauka. Wandituma kuti ndilalikire kwa a mʼndende kuti amasulidwe ndi kwa osaona kuti apenyenso, kumasulidwa kwa osautsidwa,
Omwoyo gwa Latabhugenyi guli ingulu yani, kulwokubha anyitilie amfuta okusimula emisango jo bhwana ku bhataka. Antumile okulasha okusulumulwa kwa bhanu bhabhoelwe, nokukola bhanu bhatakulola bhabhone okulola lindi. Okubhokola bhanu abhaijmibhwa bhasige ojimibhwa,
19 ndi kulalikira za nthawi imene Ambuye adzakomere mtima anthu awo.”
Okulashaomwaka gunu Latabhugenyi kolesha obhwekisi bhwae.”
20 Kenaka Iye anatseka bukulo, nalibwezera kwa wotumikira ndipo anakakhala pansi. Maso a aliyense mʼsunagogemo anali pa Iye,
Namala nafumbika echitabho, namusubhisha omutangasha we likofyanyisho, nenyanja ansi. Ameso gabhanu bhona bhanu bhaliga bhali mulikofyanyisho nibhamulola omwene.
21 ndipo anawawuza kuti, “Lero malemba awa akwaniritsidwa mmene mwamveramu.”
Namba okuloma nabho naikati, Lelo elyandiko linu lyakumila mumatwi gemwe.”
22 Onse anayankhula zabwino za Iye ndipo anadabwa ndi mawu ogwira moyo amene anatuluka mʼkamwa mwake. Iwo anafunsa kuti, “Kodi uyu si mwana wa Yosefe?”
Bhuli munu aliya amenyele chinu Yesu aliga naika, na bhamfu amwi yebhwe bhalugusibhwe na magambo go bhwengeso ganu gasokaga mukanwa kae. Bhaliga nibhaikati”unu atali mwana wa Yusufu, jitali kutyo?”
23 Yesu anawawuza kuti, “Zoonadi, mudzandiwuza mwambi uwu: Singʼanga, dzichiritse wekha! Chitanso mʼmudzi wa kwanu kuno zimene ife tamva kuti Iwe unazichita ku Kaperenawo.”
Yesu nabhabhwilati,”chimali omuja okwaika olugani lunu kwanye ati, Omuwosha, ikisha awe omwene. Chonachona chonguhye nukola Kapelinaumu, nuchikole anu muchijiji chao.”
24 Iye anapitiriza kuti, “Zoonadi, ndikukuwuzani kuti palibe mneneri amene amavomerezedwa ku mudzi kwawo.
Nalindi naikati,”chimali enibhabhwila emwe ati, atalio mulagi unu abhamwikilisha muchalo chae.”
25 Ine ndikukutsimikizirani kunali amayi ambiri amasiye mu Israeli mʼnthawi ya Eliya, kumwamba kutatsekedwa kwa zaka zitatu ndi theka ndipo kunali njala yayikulu mʼdziko lonselo.
Tali enibhabhwila emwe echimli ati bhaliga bhalio abhagasi bhamfu bhanu bhaliga bhafwilile na bhalume mu Isilaeli omwanya gwa Eliya, omwanya gunu olwile lwafungilwe ngubha kugwa payi kwo mwanya gwa miyaka esatu na nusu, anu yabheewo injala nyafu muno mu chalo chona.
26 Komabe Eliya sanatumidwe kwa mmodzi mwa iwo, koma kwa mkazi wamasiye wa ku Zerefati ku chigawo cha Sidoni.
Tali Eliya atatumilwe ku umwi wabho, tali ku kuumwi unu aliga ali Seleputa ayeyi no musi gwa Sidoni.
27 Ndipo kunali akhate ambiri ku Israeli mʼnthawi ya mneneri Elisa, koma panalibe mmodzi mwa iwo anachiritsidwa kupatula Naamani wa ku Siriya.”
Nalindi bhaliga bhalio abhagenge bhamfu mu Isilaeli mu mwanya gwao mulagi Elisha, tali atabheeo hata umwi unu eulisibhwe tali Naamani omunu wa Siliya.
28 Anthu onse mʼsunagogemo anapsa mtima atamva izi.
Abhanu bhona munda ye likofyanyisho nibhejula na lisungu bhejile bhwongwa ejo jona.
29 Anayimirira namutulutsira kunja kwa mzindawo, ndipo anamutengera pamwamba pa phiri pamene mzindawo unamangidwapo, ndi cholinga chakuti amuponyere ku phompho.
Bhemeleguyu nibhamuulusha anja yo musi, nibhamtangasha okukinga kubhenenelo bhe chima cho musigunu gwombakilwe ingulu yae, koleleki bhamwese ansi.
30 Koma Iye anangoyenda pakati pa gulu la anthulo nachokapo.
Tali alabhileo agati yebhwe naja jae.
31 Kenaka Iye anapita ku Kaperenawo, mudzi wa ku Galileya, ndipo pa Sabata anayamba kuphunzitsa anthu.
Neya natebhela Kapelenaumu, mumusi gwa Galilaya. Isabhato imwi aliga neigisha abhanu Munda ya lisomelo.
32 Iwo anadabwa ndi chiphunzitso chake chifukwa uthenga wake unali ndi ulamuliro.
Nibhalugula kulwameigisho gae, kulwokubha eigisishe ku lwo bhutulo.
33 Mʼsunagogemo munali munthu wogwidwa ndi mzimu woyipa. Iye analira ndi mawu akulu, akuti
Olusiku olwo Munda ye likofyanyisho, aligaalio omunu wa musabwa mubhibhi, alilile kwo bhulaka bhwa ingulu,”
34 “Aa! Kodi mukufuna chiyani kwa ife, Yesu wa ku Nazareti? Kodi mwabwera kudzatiwononga? Ndikudziwa kuti ndinu ndani, ndinu Woyerayo wa Mulungu!”
Chili naki nawe, Yes wa Najaleti? waja okuchisimagisha? Enimenya awe nawega! Awe nawe omwelu wa Nyamuanga!”
35 Yesu anachidzudzula kwambiri nati, “Khala chete! Tuluka mwa iye.” Chiwandacho chinamugwetsa munthuyo pansi pamaso pa onse ndipo chinatuluka wosamupweteka.
Yesu nagonya omusabwa nagubhwilati,”Jibhila Jibhila na umusokemo omunu unu!”Omusabwa ogwo nigumubha ansi agati yebhwe, gwamusokeleko bila kumukolela bhusasi bhwonabhwona.
36 Anthu onse anadabwa ndipo anati kwa wina ndi mnzake, “Kodi chiphunzitso ichi ndi chotani? Ndi ulamuliro ndi mphamvu Iye akulamulira mizimu yoyipa ndipo ikutuluka!”
Abhanu bhona nibhalugula, nibhagendelela okuloma omusango ogwo bhuli munu no wejabho. Nibhaika,”ni magamboki ganu?”Kalagilila amasabwa kwo bhuinga na manage nigabhasokako.”
37 Ndipo mbiri yake inafalikira madera onse ozungulira.
Kulwejo, jinkuma ja Yesu nijiswila bhuli mbala okwiinda omukowa ogwo.
38 Yesu anatuluka mʼsunagoge ndipo anapita kwa Simoni. Tsopano mpongozi wake wa Simoni amadwala malungo akulu, ndipo anamupempha Yesu kuti amuthandize.
Neya Yesu nasokamo mumusi omwo nengila munyumba ya Simoni. Oli, nyabhuko war Simoni aliga Ali nomuswija mwamfu, nibhamulembeleja ingulu yae.
39 Ndipo anawerama nadzudzula malungowo ndipo anamusiya. Anadzuka nthawi yomweyo nayamba kuwatumikira.
Kulwejo, Yesu namufogelela, nagonya omuswija ogwo na nigumusokako. Awo nawo nemelegulu namba okubhafulubhendela.
40 Pamene dzuwa linkalowa, anthu anabweretsa kwa Yesu onse amene anali ndi matenda osiyanasiyana, ndipo atasanjika manja ake pa aliyense, anachiritsidwa.
Lisubha lyejile lyagwa, Abhanu nibhamulembeleja Yesu bhuli munu unu abhaga no mulwae wa malwala ga bhuli mbaga. Nabhatako amabhoko gae ingulu yebhwe na nabhaosha bhona.
41 Komanso ziwanda zinkatuluka mwa anthu ambiri, zikufuwula kuti, “Inu ndinu Mwana wa Mulungu!” Koma Iye anazidzudzula ndipo sanazilole kuyankhula chifukwa zimadziwa kuti Iye ndi Khristu.
Amasambwa gona gabhasokeleko bhamfu nigasekana nigaikati,”Awe nawe omwana wa Nyamuanga!”Yesu nagonya amasabwa na atagekilisishe gaike, kulwokubha gamenyele ati omwene niwe Kilisto.
42 Kutacha, Yesu anapita ku malo a yekha. Anthu ankamufunafuna Iye ndipo pamene anafika kumene anali, anthuwo anayesetsa kumuletsa kuti asawachokere.
Bhwejile obhwile bhwela, naja mulubhala lunu atabhaoga munu. Amekofyanya ga bhanu bhaliga nibhamulembeleja na nibhaja anualigali. Nibhenda okumwingilila atajakugenda Kula nabho.
43 Koma Iye anati, “Ine ndikuyenera kulalikira Uthenga Wabwino wa ufumu wa Mulungu ku mizinda inanso chifukwa ichi ndi chimene ananditumira.”
Nawe nabhabhwila ati,”Nibhusibhusi nilashe emisango jo bhwana ejobhukama bhwa Nyamuanga mumisi ejindi myamfu, kulwokubha inu niyo injuno inu nitumilwe Anu.”
44 Ndipo Iye anapitirirabe kulalikira mʼmasunagoge a ku Yudeya.
Neya nagendelesha okulasha Munda ya amekofyanyisho mu bhuyaudi Yona.