< Luka 3 >

1 Mʼchaka cha 15 mu ulamuliro wa Tiberiyo Kaisara, Pontiyo Pilato ali bwanamkubwa wa Yudeya, Herode ankalamulira ku Galileya, mʼbale wake Filipo ankalamulira ku Iturea ndi ku dera la Trakoniti, ndipo Lusaniyo ankalamulira ku Abilene.
Itungli myaka Ikumi na utano utemi wanywa kaikani Tiberia, Matungo Pontio Pilato mudimi wang'wa Uyahudi, Herode ayi mukulu wa kisali Galilaya, Filipo muluna akwe amukulu wakisali kang'wa Iturea nutrakoniti, nu Lisania amukulu wakisali kang'wa Abilene,
2 Inalinso nthawi ya mkulu wa ansembe wa Anasi ndi Kayafa, pamene mawu a Mulungu anabwera kwa Yohane mwana wa Zakariya mʼchipululu.
Matungo umudimi mukulu wa Anasi nukayafa, Lukani Langwi Itunda alumuzie Yohana wana ang'wa Zakaria mumbuga.
3 Iye anapita ku dziko lonse lozungulira mtsinje wa Yorodani, nalalikira ubatizo wa kulapa ndi kukhululukidwa kwa machimo.
Aulongoe muhinzo mkisali kihii nikipilimiye umongo wa mazi nu ang'wa Yordani, akizitanatia itai naubadisigwa nanukuheja imilandu.
4 Monga analembera mʼbuku la Yesaya mneneri kuti: “Mawu a wofuwula mʼchipululu, konzani njira ya Ambuye, wongolani njira zake.
Anga naiandikilwe mukitabu kankani yang'wa Isaya naauotile, ululi la muntu nakulila, nyika noneeli mukondien Inzura amukulu na munonelye Inzula akwe igoloke.
5 Chigwa chilichonse chidzadzazidwa ndipo phiri lililonse ndi mtunda uliwonse zidzasalazidwa, misewu yokhotakhota idzawongoledwa, ndi njira zosasalala zidzasalazidwa.
Makombo ihi akizulig'wa malugulu niana malugulu ihi akunoneligwa ninzula niyikunyile ikikogoolwa ninzila Yihi nimbi yikuzipigwa.
6 Ndipo anthu onse adzaona chipulumutso cha Mulungu.”
Antu ihi akuona uguni wang'wi Itunda.
7 Yohane anati kwa magulu a anthu amene amabwera kudzabatizidwa ndi iye, “Ana anjoka inu! Anakuchenjezani ndani kuti muthawe mkwiyo umene ukubwera?
Kululo u Yohana akauila umilundo nukulunu antu au muhangile abatisigwe nugwenso uye wileli wanzoka nua uhungu nubii nyinyu na muhuguye kuumanka ubii nauzile.
8 Onetsani zipatso zakutembenuka mtima, ndipo musamanene mwa inu nokha kuti, ‘Tili nalo kholo lathu Abrahamu,’ pakuti ndikuwuzani kuti kuchokera ku miyala iyi, Mulungu akhoza kumuwutsira Abrahamuyo ana.
Leli Indiya niyipyani nitai namuleke kulunga mkati anyu kukete u Ibarahimu ingi tata witu kunsoko nimuila kuiti Itunda ukete uhumi kumuhumbula Ibalihimu ng'wana kupuma mumagwe aya.
9 Nkhwangwa ili kale pa muzu wamitengo, ndipo mtengo uliwonse umene subala chipatso chabwino udzadulidwa ndi kuponyedwa pa moto.”
Ingigwa ihengo aikwa mumili a miti kululo u muti nishawitugaa Indya ninza wite ng'wa mu moto.
10 Gulu la anthuwo linafunsa kuti, “Nanga tsono tichite chiyani?”
Sunga iantu niilundie akamukolya akalunga, i magwe aya utakile kutende ulii?
11 Yohane anayankha kuti, “Munthu amene ali ndi malaya awiri apatseko amene alibe, ndi amene ali ndi chakudya achitenso chimodzimodzi.”
Akasusha akalunga ang'wi muntu ukite nkanzu Ibili utakiwe aheje nkanzu ing'wi amupe umuya numugila nuyu nukete indya witume uu.
12 Amisonkho nawonso anabwera kudzabatizidwa. Iwo anafunsa kuti, “Aphunzitsi, ife tichite chiyani?”
Sunga iahoela mpia ikaza kubadisigwa akamuila, mumanyi kutendeuli.
13 Iye anawawuza kuti, “Musalandire moposa zimene muyenera.”
Aka aila, '' leki kuhoeli impia ni Idu kukela ni mutakile kuhoela.
14 Kenaka asilikali ena anamufunsa kuti, “Nanga ife tichite chiyani?” Iye anayankha kuti, “Musamalande ndalama moopseza ndipo musamanamizire anthu, khutitsidwani ndi malipiro anu.”
Anya nguru akamuila akalunga ause? kitumentuni?
15 Anthu ankadikira ndi chiyembekezo ndipo ankasinkhasinkha mʼmitima mwawo kuti mwina Yohane nʼkukhala Khristu.
Matungo, Iantu aiakite Insula akumulindila U-kristo kila muntu akasiga munkolo akwe kunsoko ng'wenso Kristo.
16 Yohane anayankha onse kuti, “Ine ndikubatizani ndi madzi. Koma wina wondiposa ine mphamvu adzabwera amene sindili woyenera kumasula lamba wa nsapato zake. Iyeyu adzakubatizani inu ndi Mzimu Woyera ndi moto.
U yohana akaaila ihii, ''unene kumubatiza unye kumanzi ukoli nuzile nukete uhumi kukila une, nishantakiwe kutungula uludingi la ilatu yakwe. ukumubatiza unye kung'wang'welu nu kumoto.
17 Mʼdzanja lake muli chopetera kuti ayeretse powomberapo tirigu ndi kusonkhanitsa tirigu ndipo adzatentha zotsalira zonse ndi moto wosazimitsika.”
Ipetelo lakwe likoli kumukono akwe kupyagula ni Iza ikiuga nikakupetela Ingano nukilingila Ingano misalanka lakwe ingi gwa ukuma sansa imakamilya kumoto ni shawilimaa.
18 Ndipo ndi mawu ena ambiri, Yohane anawachenjeza anthu ndi kuwalalikira Uthenga Wabwino.
Ukeneli widu autanantilye nkani ninza kuantu.
19 Koma pamene Yohane anadzudzula Herode wolamulirayo chifukwa chokwatira Herodia, mkazi wa mʼbale wake, ndi zoyipa zina zonse anazichita,
U Yohana aumpatile U - Herode mukulu wa kisali akamutina U - Herode musungu wa ng'wa muluna akwe nuku mabi nidu ni mangiza u Herode nutendile.
20 Herode anawonjezanso choyipa ichi pa zonsezo: Anatsekera Yohane mʼndende.
Matungo naitwile Herde aiwitumile uubi ukulu na ngulu, akamu tunga Yohana kukitungo.
21 Pamene anthu onse ankabatizidwa, Yesu anabatizidwanso. Ndipo akupemphera, kumwamba kunatsekuka.
Ingi aipumie matungo iantu ihii naiakubadilisi gwa nu Yesu nu ng'wenso aubadisigwe, Imatungo naukulompa, Ilunde likalunguka.
22 Mzimu Woyera anatsika pa Iye mumaonekedwe a nkhunda ndipo mawu anamveka kuchokera kumwamba: “Iwe ndiwe Mwana wanga wokondedwa; ndimakondwera nawe.”
Ung'wa ngwelu akasima migulya akwe. anga Inyunyi, Matungo yayo yayo luli likaza kupuma milunde likalilya. Ue Ingi nu anso ng'wana wane ninumukuilye.
23 Ndipo Yesu anali ndi zaka makumi atatu pamene anayamba ntchito yake. Monga mmene anthu ankaganizira, Iyeyo anali mwana wa Yosefe, mwana wa Heli,
U-Yesu ung'wenso, naiwapisha Imyaka makumi ataatu. Akandilya kumanyisa akazimpaya nigwa anga ng'wana ang'wa Yusufu, anga Eli.
24 mwana wa Matate, mwana wa Levi, mwana wa Meliki, mwana wa Yaneyi, mwana wa Yosefe
Ni ang'wi akalunga ng'wana wa ng'wa Mathati, ng'wana wang'wa Lawi, ng'wana wang'wa Melki, ng'wana wa ng'wa Yona, ng'wana wang'wa Yusufu.
25 mwana wa Matati, mwana wa Amosi, mwana wa Naomi, mwana wa Esli, mwana wa Nagai,
Ng'ana wa Matathia, ng'wana wa ng'wa Amosi ng'wana wa ng'wa Nahumu, ng'wana wa ng'wa Esli, ng'wana wa ng'wa Nagai.
26 mwana wa Maati, mwana wa Matatiyo, mwana wa Simeoni, mwana wa Yosefe, mwana wa Yoda
Ng'wana wang'wa Maati, ng'wana wang'wa Matathia, ng'wana wang'wa Semein, ng'wana wang'wa Yusufu, ng'wana wang'wa Yuda.
27 mwana wa Yohanani, mwana wa Resa, mwana wa Zerubabeli, mwana wa Salatieli, mwana wa Neri,
Ng'wana wang'wa Yoanani, ng'wana wang'wa Resa, ng'wana wang'wa Zerubabeli, ng'wana wang'wa Shealtieli, ng'wana wang'wa Neri,
28 mwana wa Meliki, mwana wa Adi, mwana wa Kosamu, mwana wa Elmadama, mwana wa Ere,
ng'wana wang'wa Melki, ng'wana wang'wa Adi, ng'wana wang'wa Kosamu, ng'wana wang'wa Elmadamu, ng'wana wang'wa Eri,
29 mwana wa Jose, mwana wa Eliezara, mwana wa Yorimu, mwana wa Matati, mwana wa Levi,
ng'wana wang'wa Yoshua, ng'wana wang'wa Eliezeri, ng'wana wang'wa Yorimu, ng'wana wang'wa Matath, ng'wana wang'wa Lawi.
30 mwana wa Simeoni, mwana wa Yuda, mwana wa Yosefe, mwana wa Yonamu, mwana wa Eliakimu,
Ng'wana wang'wa Simeoni, ng'wana wang'wa Yuda, ng'wana wang'wa Yusufu, ng'wana wang'wa Yonamu, ng'wana wang'wa Eliyakimu.
31 mwana wa Meleya, mwana wa Mena, mwana wa Matata, mwana wa Natani, mwana wa Davide,
Ng'wana wang'wa Melea, ng'wana wang'wa Mena, ng'wana wang'wa Matatha, ng'wana wang'wa Nathani, ng'wana wang'wa Daudi.
32 mwana wa Yese, mwana wa Obedi, mwana wa Bowazi, mwana wa Salimoni, mwana wa Naasoni,
Ng'wana wang'wa Yese, ng'wana wang'wa Obedi, ng'wana wang'wa Boazi, ng'wana wang'wa Salmoni, ng'wana wang'wa Nashoni.
33 mwana wa Aminadabu, mwana wa Arni, mwana wa Hezronu, mwana wa Perezi, mwana wa Yuda,
Ng'wana wang'wa Abinadabu, ng'wana wang'wa Aramu, ng'wana wang'wa Hesroni, ng'wana wang'wa Peresi, ng'wana wang'wa Yuda,
34 mwana wa Yakobo, mwana wa Isake, mwana wa Abrahamu, mwana wa Tera, mwana wa Nakoro,
Ng'wana wang'wa Yakobo, ng'wana wang'wa Isaka, ng'wana wang'wa Ibrahimu, ng'wana wang'wa Tera, ng'wana wang'wa Nahori,
35 mwana wa Serugi, mwana wa Reu, mwana wa Pelegi, mwana wa Eberi, mwana wa Sela,
Ng'wana wang'wa Seruig, ng'wana wang'wa Ragau, ng'wana wang'wa Pelegi, ng'wana wang'wa Eberi, ng'wana wang'wa Sala,
36 mwana wa Kainane, mwana wa Arfaksadi, mwana wa Semu, mwana wa Nowa, mwana wa Lameki,
Ng'wana wang'wa Kenani, ng'wana wang'wa Arfaksadi, ng'wana wang'wa Shemu, ng'wana wang'wa Nuhu, ng'wana wang'wa Lameki,
37 mwana wa Metusela, mwana wa Enoki, mwana wa Yaredi mwana wa Malaleeli, mwana wa Kainane,
Ng'wana wang'wa Methusela, ng'wana wang'wa Henoko, ng'wana wang'wa Yaredi, ng'wana wang'wa Mahalalei, ng'wana wang'wa Kenani,
38 mwana wa Enosi, mwana wa Seti, mwana wa Adamu, mwana wa Mulungu.
Ng'wana wang'wa Enashi, ng'wana wang'wa Sethi, ng'wana wang'wa Adamu, ng'wana wang'wa Tunda.

< Luka 3 >