< Luka 16 >

1 Yesu anawuza ophunzira ake kuti, “Panali munthu wina wachuma amene kapitawo wake anzake anamuneneza kuti amawononga chuma chakecho.
Yesu nowachone jopuonjrene niya, “Ne nitie jamoko moro, ma ngʼat mane rito mwandune ne odonjne ni ketho gige.
2 Choncho anamuyitana ndi kumufunsa kuti, ‘Kodi nʼchiyani chimene ndikumva za iwe? Pereka tsatanetsatane wa ntchito yako, pakuti supitirizanso kukhala kapitawo wanga.’
Omiyo noluonge ire kendo nopenje ni, ‘En angʼo mawinjo kuomini? Chiw ane kwan kuom gigo duto mirito, nikech ok inyal bedo jarit giga kendo ngangʼ!’
3 “Kapitawoyo analingalira kuti, ‘Kodi tsopano ndidzachita chiyani? Bwana wanga andichotsa ntchito. Ine ndilibe mphamvu zokwanira zolimira, komanso ine ndimachita manyazi kupempha.
“Jarit noparo kende owuon ni, ‘Abiro timo angʼo koro? Ruodha koro maya tija. Ok an ratego moromo ma dapur, to wiya kuot mondo akwechi.
4 Ine ndikudziwa chimene ndidzachita kotero kuti, pamene ntchito yanga yatha pano, anthu adzandilandire mʼnyumba zawo.’
Angʼeyo gima abiro timo, ma ka aweyo tich ka, to ji biro rwaka utegi!’
5 “Choncho iye anayitana aliyense amene anali ndi ngongole kwa bwana wake. Iye anafunsa woyamba, ‘Kodi uli ndi ngongole yotani kwa bwana wanga?’
“Omiyo noluongo jogope ruodhe achiel achiel. Nopenjo mokwongo ni, ‘In-gi gowi mar ruodha marom nadi?’
6 “Iye anayankha kuti, ‘Migolo yamafuta a olivi 800.’ “Kapitawo uja anamuwuza iye, ‘Tenga pamene unalemba ngongole yakoyo, khala pansi msanga ndipo lemba kuti ndi migolo 400.’
“Nodwoke ni, ‘Debe mia aboro mag mo.’ “Jarit tich nowachone ni, ‘Bed piny piyo piyo, ikaw kitapi indikie ni, mia angʼwen.’
7 “Kenaka iye anafunsa wachiwiri kuti, ‘Nanga iwe uli ndi ngongole yotani?’ “Iye ayankha kuti madengu a tirigu 1,000. “Iye anati, ‘Tenga pamene unalemba ngongole yakoyo ndipo ulembepo 800.’
“Eka nopenjo ngʼat mar ariyo ni, ‘In to, gopi oromo adi?’ “Nodwoke ni, ‘Gunia alufu achiel mag ngano.’ “Nowachone ni, ‘Kaw kitapini, indike ni mia aboro.’
8 “Bwana anayamikira kapitawo wosakhulupirikayo popeza anachita mochenjera. Pakuti anthu a dziko lino lapansi ndi ochenjera kwambiri akamachita zinthu ndi anthu ofanana nawo kuposa anthu a kuwunika. (aiōn g165)
“Ruoth nopako jarit gige ma ok kareno nikech notiyo gi rieke. Nimar jopinyni ongʼeyo tiyo mariek gi jowadgi moloyo jogo mawuotho e ler. (aiōn g165)
9 Ine ndikukuwuzani inu, gwiritsani ntchito chuma cha dziko lapansi kuti mudzipezere nokha abwenzi, kuti pamene chatha mudzalandiridwe mʼmalo okhala amuyaya. (aiōnios g166)
Awachonu ni tiuru gi mwandu mag piny mondo umakgo osiepe ne un uwegi, mondo ka chiengʼ ma mwandugo orumo, norwaku e kar dak mochwere. (aiōnios g166)
10 “Amene akhulupirika pa zinthu zochepa akhoza kukhulupirikanso pa zinthu zambiri, ndipo amene sakhulupirika pa zinthu zochepa adzakhala wosakhulupirika pa zinthu zambiri.
“Ngʼat minyalo geno gi gima tin, inyalo gene bende gi gik mangʼeny, to ngʼat ma ok ja-adiera gi gima tin bende ok nyal bedo ja-adiera gi gik mangʼeny.
11 Ndipo ngati simunakhale okhulupirika pogwiritsa ntchito chuma cha dziko lapansi, ndani amene adzakusungitsani chuma chenicheni?
Emomiyo ka ok usebedo jo-adiera e tiyo gi mwandu mar pinyni, en ngʼat mane mabiro genou gi mwandu madier?
12 Ndipo ngati simunakhale okhulupirika ndi chuma cha mwini wake, ndani amene adzakupatsani katundu wanuwanu?
To ka ok usebedo jo-adiera gi mwandu ngʼat machielo, en ngʼat mane madimiu mwandu ma maru uwegi?
13 “Palibe wantchito amene angatumikire mabwana awiri. Mwina iye adzadana ndi wina ndi kukonda winayo, kapena adzakhala wodzipereka kwa wina ndi kumunyoza winayo. Inu simungathe kutumikira Mulungu komanso ndalama nthawi imodzi.”
“Onge jatich manyalo tiyo ne ruodhi ariyo. Nimar obiro chayo achiel to ohero machielo, kata obiro chiwore ne achiel to ochayo machielo. Ok inyal tiyo ne Nyasaye kendo ne pesa.”
14 Afarisi amene ankakonda ndalama atamva zimenezi anamuseka Yesu.
Jo-Farisai mane ohero pesa nowinjo magi duto kendo neginyiero kagijaro Yesu.
15 Yesu anawawuza kuti, “Inu ndi amene mumadzilungamitsa nokha pamaso pa anthu, koma Mulungu amadziwa mitima yanu. Zinthu zimene anthu amaziyesa zopambana, ndi zonyansa pamaso pa Mulungu.
Nowachonegi niya, “Un ema utimoru joma kare e wangʼ ji, to Nyasaye ongʼeyo chunyu. Gima okaw ni ber ahinya gi ji, kuom Nyasaye en gima kwero.
16 “Malamulo ndi Aneneri zinagwira ntchito mpaka nthawi ya Yohane. Kuyambira nthawi imeneyo, Uthenga Wabwino wa ufumu wa Mulungu ukulalikidwa, ndipo aliyense akuyesetsa mwamphamvu kuti alowemo.
“Chik kod Jonabi ne nigi teko nyaka chop ndalo mar Johana. Chakre kanyo, Injili mar pinyruoth Nyasaye osebedo kilando, kendo ngʼato ka ngʼato riyore mondo odonjie.
17 Nʼkwapafupi kuti kumwamba ndi dziko lapansi zichoke kulekana ndi kuti kalemba kakangʼono kachoke mʼMalamulo.
To yot mondo polo gi piny orum, moloyo ka nukta achiel matinie moloyo olal kuom Chik.
18 “Aliyense amene asiya mkazi wake ndi kukakwatira mkazi wina akuchita chigololo, ndipo mwamuna amene akwatira mkazi wosiyidwayo akuchitanso chigololo.”
“Ngʼato mowere gi chiege mokendo dhako machielo, odonjo e richo mar terruok, to ngʼat mokendo dhako ma chwore oweyo, bende odonjo e richo mar terruok.
19 “Panali munthu wachuma amene ankavala zovala zofiirira za mtengowapatali ndipo ankakhala moyo wachisangalalo tsiku lililonse.
“Ne nitie jamoko moro mane rwako lewni mokikore kod lewni mayom ma nengogi tek, kendo nodak e ngima mamalo mar mor ndalo duto.
20 Pa khomo la mpanda wake ankagonekapo munthu wopempha wotchedwa Lazaro, wazilonda thupi lonse
E dhorangaye noketie jakwecho miluongoni Lazaro, ma adhonde nopongʼo dende
21 ndipo ankafunitsitsa atadya zomwe zinkagwa pansi kuchokera pamene munthu wolemerayo amadyerapo. Agalu ankabweranso ndi kumanyambita zilonda zake.
kendo nogombo chamo ngʼinjo molwar e bwo mesa jamokono. Kata mana guogi bende ne biro minangʼ adhondene.
22 “Nthawi inafika imene wopemphayo anamwalira ndipo angelo anamunyamula nakamuyika mʼmanja mwa Abrahamu. Munthu wolemerayo anamwaliranso ndipo anayikidwa mʼmanda.
“Sa nochopo ma jakwechono notho kendo malaika notingʼe, otere e bath Ibrahim. Jamoko bende notho kendo noyike.
23 Ali mʼgehena kuzunzika, anakweza maso ake ndipo anaona Abrahamu ali ndi Lazaro pambali pake. (Hadēs g86)
Kane en e Piny Joma otho kisande malit, nongʼiyo malo to noneno Ibrahim gi kuma bor kod Lazaro e bathe. (Hadēs g86)
24 Ndipo anafuwula kwa iye kuti, ‘Abambo Abrahamu, mundimvere chisoni ine ndipo mutumeni Lazaroyo kuti aviyike msonga ya chala chake mʼmadzi kuti aziziritse lilime langa, chifukwa ndikumva ululu mʼmoto muno.’
Omiyo noluonge kowacho niya, ‘Wuora Ibrahim kecha kendo or Lazaro olut lith lwete e pi mondo okwena lewa, nikech an-gi rem malit e ligek majni.’
25 “Koma Abrahamu anayankha kuti, ‘Mwanawe kumbukira kuti nthawi yamoyo wako unalandira zinthu zako zabwino, pamene Lazaro analandira zinthu zoyipa, koma tsopano akusangalatsidwa kuno ndipo iwe uli mʼmazunzo.
“To Ibrahim nodwoke ni, ‘Wuoda, parie ni e ndalo mar ngimani ne iyudo gik mabeyo, ka Lazaro to ne yudo gik maricho, to koroni oneno maber ka eri, to in inie rem malit.
26 Ndipo kuwonjezera pa zonsezi, pakati pa inu ndi ife pali chiphompho chachikulu chimene chinayikidwa, kotero kuti amene akufuna kubwera kumeneko sangathe, kapena palibe amene angawoloke kuchokera kumeneko kudzafika kuno.’
To bende moloyo ne mano duto, e kindwa kodi nitie hoho mangʼongo moseketi, mondo otam jogo madwaro aa ka obi iru kata ngʼato ok nyal ngʼado oa koru obi irwa koni.’
27 “Iye anayankha kuti, ‘Ndipo ndikupemphani inu, abambo, mutumeni Lazaro ku nyumba ya abambo anga,
“Nodwoko ni, ‘Koro akwayoi, wuora, or Lazaro odhi od wuora,
28 pakuti ine ndili ndi abale asanu. Lolani iye akawachenjeze kotero kuti asadzabwere kumalo ano amazunzo.’
nimar an-gi owetena abich. Odhiyo osiemgi, mondo kik gin bende gibi e kar sand malitni.’
29 “Abrahamu anayankha kuti, ‘Ali ndi Mose ndi Aneneri; aleke amvere iwo.’
“Ibrahim nodwoke ni, ‘Gin kod Musa gi Jonabi, owinjore giwinjgi.’
30 “Iye anati, ‘Ayi, bambo Abrahamu, koma ngati wina ochokera kwa akufa adzapita kwa iwo, adzatembenuka mtima.’
“Nowacho ni, ‘Ooyo wuonwa Ibrahim, to ka ngʼato oa kuom joma otho modhi irgi, to gibiro weyo richo.’
31 “Anati kwa iye, ‘Ngati iwo samvera Mose ndi Aneneri, sadzakhulupirira ngakhale wina atauka kwa akufa.’”
“Nowachone ni, ‘Ka ok ginyal winjo Musa gi Jonabi, ok ginyal yie winjo kata ngʼato mochier oa kuom joma otho.’”

< Luka 16 >