< Luka 14 >

1 Pa tsiku lina la Sabata, Yesu atapita kukadya ku nyumba ya Mfarisi wodziwika, Afarisi anamulonda mosamalitsa.
Lyubha limo lya Pumulila a Yeshu bhashinkwenda kulya shalya kumui kwa akalongolele bhamo bha Mapalishayo, bhandunji bhapalinji penepo gubhaalolesheyenje kwa kaje.
2 Poteropo, patsogolo pake panali munthu amene anadwala matenda otupa mimba ndi miyendo.
Mmujo jabho a Yeshu ashinkupagwa mundu nnwele shitaka.
3 Yesu anafunsa Afarisi ndi akatswiri amalamulo kuti, “Kodi ndi zololedwa kuchiritsa pa tsiku la Sabata kapena ayi?”
A Yeshu gubhaabhushiyenje bhaajiganya bha shalia na Mapalishayo, “Ilipinjikwa eu ikapinjikwa kunnamya mundu Lyubha lya Pumulila?”
4 Koma iwo sanayankhe. Tsono atamutenga munthuyo, Iye anamuchiritsa ndipo anamuwuza kuti azipita.
Ikabheje bhanganya bhala gubhatemingene ilili. A Yeshu gubhankamwile nnwele jula gubhannamiye, gubhanneshile aijabhulile.
5 Kenaka Iye anawafunsa kuti, “Kodi ngati mmodzi mwa inu ali ndi mwana wamwamuna kapena ngʼombe imene yagwera mʼchitsime tsiku la Sabata, kodi simungamuvuwulemo tsiku lomwelo?”
Kungai gubhaabhushiye, “Munkumbi gwenunji gani mwanagwe eu ng'ombe jwakwe atumbushilaga nniiko, akananshoye pabha Lyubha lya Pumulila?”
6 Ndipo iwo analibe choyankha.
Ikabheje bhangakombolanga kwajaangula.
7 Iye ataona momwe alendo amasankhira malo aulemu pa tebulo, Iye anawawuza fanizo ili:
A Yeshu bhakaabhonanjeje bhashemilwenje bhala shibhatendaga kwiagulilanga itengu ya mmujo, gubhaalugulilenje.
8 “Pamene wina wakuyitanani ku phwando la ukwati, musakhale pa malo aulemu ayi, chifukwa mwina anayitananso munthu wina wolemekezeka kuposa inu.
“Ibhaga mundu anshemaga kundoa, nnatame pa shitengu sha mmujo, inabha apali juna ashemilwe jwa kupunda mmwe.
9 Ngati zitatero, ndiye kuti munthu uja amene anakuyitani inu nonse awiri adzakuwuzani kuti, ‘Mupatseni munthu uyu malo anu.’ Pamenepo inu mudzachita manyazi, pokakhala malo wotsika.
Bhanshemilenje bhala shibhajiye kummalanjila, ‘Mwaapiye abha.’ Penepo nkupinga kola oni pa bhandu bhowe nnikwendatama shitengu sha nnyuma.
10 Koma akakuyitanani, khalani pa malo otsika, kuti amene anakuyitanani uja adzakuwuzeni kuti, ‘Bwenzi, bwera udzakhale pa malo aulemu pano.’ Pamenepo inu mudzalandira ulemu pamaso pa alendo anzanu onse.
Ikabhe nshemwaga ntame shitengu sha nnyuma, nkupinga nnyene nyumba ajiyaga annugulile, ‘Ambwiga, nnjiye mmujo muno.’ Penepo nkupinga ishimiywa na bhowe bhatemingene pamo na mmwe.
11 Pakuti aliyense wodzikuza adzamuchepetsa, ndipo aliyense wodzichepetsa adzamukweza.”
Pabha, jojowe akwiikweya apinga tuluywa, na akwiituluya apinga kweywa.”
12 Kenaka Yesu anati kwa mwini malo uja, “Ukakonza chakudya chamasana kapena chamadzulo, usamayitane abwenzi ako, abale ako, anthu afuko lako kapena anzako achuma; ngati iwe utero, iwo adzakuyitananso, choncho udzalandiriratu mphotho yako.
Kungai gubhaabhalanjile na bhashemile bhala, “Punkuteleka kalamu ibhe mui eu shilo, nnaashemanje ashaambwiga ajenu eu ashaalongo ajenu eu ashaatami ajenu bhalinginji matajilipe, na bhalabhonji bhana kwiya kunshemanga nibha nnipilwe yumwaatendelenje ila.
13 Koma ukakonza phwando, itana anthu osauka, ofa ziwalo, olumala ndi osaona.
Ikabheje, punkuteleka kalamu, mwaashemanje bhaalaga, bhaalemalanga na ashinangwabha na ashinangalole,
14 Pamenepo udzakhala wodala, chifukwa iwo sangakubwezere kanthu, koma Mulungu ndiye adzakubwezera pa chiukitso cha olungama.”
na mmwe shimpate mboka, pabha bhene bhanganyabho bhangalinginji sha kunnipa. A Nnungu shibhampe upo yenu lyubha lishibhayukanje bhandunji bhakwetenje aki.”
15 Mmodzi mwa amene amadya naye atamva izi, anati kwa Yesu, “Ndi wodala munthu amene adzadye nawo mu ufumu wa Mulungu.”
Mundu jumo munkumbi gwa bhatemingene na a Yeshu pa shalya gwashite, “Mbaya jwene mundu shalye kalamu mu Upalume gwa a Nnungu.”
16 Yesu anayankha kuti, “Munthu wina ankakonza phwando lalikulu ndipo anayitana alendo ambiri.
A Yeshu gubhannjangwile, “Bhandu bhamo bhashinkuteleka kalamu jikulungwa, gubhaashemilenje bhandunji bhabhagwinji.
17 Nthawi yaphwando itakwana anatuma wantchito wake kuti akawuze onse amene anayitanidwa kuti, ‘Bwerani, pakuti zonse zakonzeka.’
Lyubha lya kalamu likaishileje gubhantumile ntumishi jwabho akaalugulilanje bhashemilwenje bhala kuti, ‘Nnjiyangane, indu yowe ili tayali.’
18 “Koma onse anayamba kupereka zifukwa mofanana. Woyamba anati, ‘Ine ndangogula kumene munda, ndipo ndikuyenera kupita kuti ndikawuone. Pepani mundikhululukire.’
Ikabheje bhowe, gubhatandwibhenje kwiilugula jumo jumo. Jwa ntai gwashite, ‘Njigombola nngunda, kwa nneyo ngunapinjikwa nyende ngaulole shonde bhai, uneshe nyende.’
19 “Wina anati, ‘Ndangogula kumene ngʼombe khumi zokoka ngolo ndipo kupita kukaziyesa. Pepani mundikhululukire.’
Na juna gwashite, ‘Njigombola ng'ombe ya lima, majela nng'ano, kwa nneyo ngunakwenda kwiilinga, shonde bhai uneshe nyende.’
20 “Wina anatinso, ‘Ine ndangokwatira kumene, choncho sinditha kubwera.’
Na juna gwashite, ‘Njilomba, kwa nneyo ngaika.’
21 “Wantchitoyo anabwera ndikudzamuwuza bwana wakeyo zimenezi. Pamenepo mphwandoyo anapsa mtima ndipo analamula wantchito wakeyo kuti, ‘Pita msangamsanga kunja mʼmisewu ndi mʼmakwalala a mu mzinda ndipo ukabweretse osauka, ofa ziwalo, osaona ndi olumala.’
“Ntumishi jula gwabhujile nigwabhalugulile bhakulungwa bhakwe jene nganijo. Bhayene nyumba bhala gubhatumbele, gubhannugulile ntumishi jwabho, ‘Ujende shangu kumpanda njindo na mmipanda ja pa shilambo pano, ujiyenabhonji nnyumba muno bhalaga, na ashinangwabha, na ashinangalole, na bhaalemalanga.’
22 “Wantchitoyo anati, ‘Bwana, zimene munanena zachitika koma malo akanalipobe.’
Kungai ntumishi jula gwashite, ‘Mmakulungwa, innajile ila ndendile, ikabheje mwaatama mwatangu.’
23 “Ndipo mbuye uja anawuza wantchito wake kuti, ‘Pita kunja ku misewu ikuluikulu ndi kunja kwa mpanda ndipo ukawawuze kuti alowe, kuti nyumba yanga idzaze.
Bhakulungwa bhala gubhannugulile ntumishi jula, ‘Ujende mmipanda njindo na mipanda ja pa shilambo pano ukaashishilishiyanje bhandunji bhajiyangane, nyumba jangu jigumbale.
24 Ine ndikukuwuzani inu kuti palibe ndi mmodzi yemwe mwa anthu amene anayitanidwa adzalawa phwandolo.’”
Ngunakummalanjilanga mmowe kuti, jwakwapi nkali jumo munkumbi gwa bhunaashemilenje gwantai bhala shapaye shalya shangu.’”
25 Gulu lalikulu la anthu linkayenda naye Yesu ndipo atatembenukira kwa iwo anati,
Penepo, likukute likulungwa lya bhandu gulilongene na a Yeshu. Bhai, gubhaatendebhushilenje bhandunji gubhaalugulilenje,
26 “Ngati wina aliyense abwera kwa Ine ndipo sadana ndi abambo ndi amayi ake, mkazi wake ndi ana, abale ake ndi alongo ake, inde ngakhale moyo wake omwe, iye sangakhale ophunzira wanga.
“Mundu jojowe apinga kubha nkujiganywa jwangu ambinje, kupunda shakutikwaapinga ainagwe na akwabhe na akagwe na ashibhanagwe, na ashaapwakwe na ashaalumbugwe na nkali kupunda shakuti kwiipinga nnyene.
27 Ndipo aliyense amene sasenza mtanda wake ndi kunditsata Ine sangakhale ophunzira wanga.
Mundu akaujigale nshalabha gwakwe ningagula akakombola kubha nkujiganywa jwangu.”
28 “Taganizani, ngati wina mwa inu akufuna kumanga nsanja, kodi iye sayamba wakhala pansi ndi kuganizira za mtengo wake kuti aone ngati ali ndi ndalama zokwanira kuti atsirizire?
Pabha, gani munkumbi gwenunji apingaga kushenga nnala, akatandubha kutama nilola galama jakwe nkupinga amumanye ibhaga akwete mmbiyaya malila?
29 Pakuti ngati ayika maziko ndi kulephera kutsiriza, aliyense amene adzayiona adzamuseka,
Inabha atandubhaga kushenga nshingi niilepela kumaliya, bhandunji shibhalolanjebho shibhanng'ekanje,
30 nanena kuti, ‘Munthu uyu anayamba kumanga koma sanathe kutsiriza.’
bhalinkutinji. Aju munduju atandwibhe kushenga, ikabheje ashilepela malishiya.
31 “Kapena mfumu imene ikupita ku nkhondo kukamenyana ndi mfumu ina, kodi siyamba yakhala pansi ndi kulingalira ngati ingathe ndi anthu 10,000 kulimbana ndi amene akubwera ndi 20,000?
Eu mpalume jwashi apinga kwenda komana na upalume guna, anatandubhe kutama ni niganishiya ibhaga shakombole na ashimanjola bhakwe elupu likumi limo, kwenda komana na a mpalume bhakwete manjola elupu makumi gabhili?
32 Ngati singathe, idzatuma nthumwi pomwe winayo ali kutali ndi kukapempha mgwirizano wamtendere.
Abhonaga akakombola, shatume ntenga kupinga ulele bhakanabhe bhandishila.
33 Mʼnjira yomweyo, wina aliyense wa inu amene sasiya zonse ali nazo sangakhale ophunzira wanga.
Bhai nneyo peyo, akapagwa nkali jumo munkumbi gwenunji apingabha nkujiganywa jwangu, akaleshe indu yowe yakwete.
34 “Mchere ndi wabwino, koma ngati usukuluka adzawukoleretsanso ndi chiyani?
“Nnjete ni ja mmbone, ibhaga jikanonye, jitagwe nndi jinonye kabhili?
35 Suyeneranso ngakhale mʼnthaka kapena kudzala la manyowa; umatayidwa kunja. “Amene ali ndi makutu akumva, amve.”
Jikapwaa kwa litaka wala kwa tenda mbolela. Ikabheje pakujijaa kwa taliya. Akwete makutujo apilikane!”

< Luka 14 >