< Luka 13 >
1 Nthawi yomweyo panali ena amene analipo omwe amamuwuza Yesu za Agalileya amene magazi awo Pilato anawasakaniza ndi nsembe zawo.
Kumwanya ogwo abhanu nibhamubhwila ingulu ya Abhagalilaya bhanu Pilato etile no okusasha amanyinga gebhwe ne ebhitambo bhyebhwe.
2 Yesu anayankha kuti, “Kodi mukuganiza kuti Agalileya amenewa anali ochimwa kwambiri kuposa Agalileya ena onse chifukwa anavutika mʼnjira iyi?
Yesu nabhasubhya nabhabhwila ati, “Omwitogela ati Abhagalilaya abho bhaliga bhali ne ebhibhi okukila Abhagalilaya abhandi bhona ati nicho chakola bhabhone amabhibhi ago?
3 Ine ndikuti, ayi! Koma ngati inu simutembenuka mtima, inunso mudzawonongeka nonse.
Pai, enibhabhwila ati, nawe emwe ona mukabhula okuta, emwe ona omusingalika kutyo.
4 Kapena anthu 18 aja amene anafa nsanja ya Siloamu itawagwera, kodi mukuganiza kuti iwo aja anali ochimwa kwambiri kuposa onse amene amakhala mu Yerusalemu?
Amo bhaliya bhanu ekumi na munana eliya Siloamu bhanu bhagwiliwe no echisonge nigubheta, omwiganilisha ati bhaliga bhana ebhibhi kukila abhanu bhandi mu Yersalemu?
5 Ine ndikuti, ayi! Koma ngati inu simutembenuka mtima, inunso mudzawonongeka nonse.”
Pai, anye enaika ati, nawe mukabhula okuta, emwe ona omusingalika.
6 Kenaka Iye anawawuza fanizo kuti, “Munthu wina anali ndi mtengo wamkuyu, umene anadzala mʼmunda wamphesa, ndipo Iye anapita kukayangʼana zipatso, koma sanazipeze.
Yesu nabhabhwila echijejekanyo chinu, “Omunu umwi aliga ayambile liti lyo mtini mwisambu lyae, neya najokulolako amatwasho kwiti okwo nawe atagabhwene.
7 Tsono kwa munthu amene amasamalira munda wamphesawo anati, ‘Kwa zaka zitatu tsopano ndakhala ndikubwera kudzafuna chipatso pa mtengo uwu ndipo sindinachipeze. Udule! Nʼchifukwa chiyani ukuwononga nthaka?’
Nabhwila unu aliga nalimilila omugunda, 'Lola kwe emyaka esatu enijaga okulegeja okulonda amatwasho kwiti kunu nawe nitagabhonako! Nuliteme. Kubhaki linyamule lisambu?
8 “Munthuyo anayankha kuti, ‘Bwana, tawusiyani kwa chaka chimodzi chokha ndipo ine ndikumba ngalande mozungulira ndi kuthira manyowa.
Oyo alimililaga omugunda nasubhya naika ati, 'nulisigeo omwaka gunu koleleki nilisejele niliteleko imboleya.
9 Ngati udzabale zipatso chaka chamawa, zili bwino! Koma ngati sudzabala, pamenepo mudzawudule.’”
Labha likatwasha omwaka gunu oguja, ni kisi; nawe labha likabhula okutwasha, uliteme!”'
10 Pa Sabata Yesu ankaphunzitsa mʼsunagoge ina,
Mbe oli, Yesu aliga neigisha mu limwi lya Amasinagogi akatungu ka Isabhato.
11 ndipo momwemo munali mayi amene anali ndi mzimu woyipa umene unamudwalitsa zaka 18. Iye anali wokhota msana ndipo samatha kuweramuka ndi pangʼono pomwe.
Lola, aliga alio omugasi umwi kwe myaka ekumi na munana aliga ali na lisambwa ebhibhi elyo obhunyoke, omugasi oyo aliga ekotele na atali na bhutulo chimwi obhwo kwimelegulu.
12 Yesu atamuona anamuyitana kutsogolo ndipo anati kwa iye, “Amayi, mwamasulidwa ku mavuto.”
Yesu ejile amulola, namubhilikila, namubhwila ati, “Mai, watesulilwa okusoka mubhunyoke bhwao.”
13 Kenaka anasanjika manja ake pa iye, ndipo nthawi yomweyo anawongoka nayamika Mulungu.
Natula amabhoko gaye ingulu yaye, achalao omubhili gwaye ngugololoka nalamya na Nyamuanga. Nawe omukulu wa lisinagogi nabhiililwa kulwokubha Yesu amuosishe kulusiku lwa Isabhato.
14 Chifukwa cha kuyipidwa kuti Yesu anachiritsa pa Sabata, wolamulira sunagoge anati kwa anthu, “Pali masiku asanu ndi limodzi ogwira ntchito. Choncho bwerani kuti mudzachiritsidwe masiku amenewo osati pa Sabata.”
Nio omwangalisi nasubhya nabhwila liijo ati, “Jilio naku mukaga ejokukolela emilimu. Muje ukuosibhwa amalwaye jinsiku ejo, musige okukola kutyo kulusiku lwa Isabhato.'
15 Ambuye anamuyankha kuti, “Iwe wachiphamaso! Kodi nonsenu simumasula pa Sabata ngʼombe zanu kapena bulu kumuchotsa mʼkhola ndi kupita naye kukamupatsa madzi?
Omukama namusubhya naika ati, “abhanafiki! atalio umwi kwimwe unu kasibhula insikili yaye amo ing'a okusoka muchigoli akaisila okunywa amanji kulusiku lwa Isabhato?
16 Nanga mayiyu, amene ndi mwana wa Abrahamu, ndipo anamangidwa ndi Satana zaka 18, kodi siwoyenera kuti amasulidwe msinga imeneyi pa tsiku la Sabata?”
Mbe omugasi unu omuasha wa Abrahamu, atengene okusulumulwa okusoka mwibhoyelo lya Shetani linu lyaliga limubhoyele myaka ekumi na munana kulusiku lwa Isabhato?
17 Atanena izi, onse omutsutsa anachititsidwa manyazi, koma anthu anakondwera ndi zodabwitsa zonse zimene Iye anazichita.
Ao aliga achaika emisango ejo, bhona bhanu bhaliga nibhamuganya nibheswala, tali liijo lyona na abhandi nibhakondelelwa ingulu ya amagambo gokulugusha ganu akolele.
18 Kenaka Yesu anafunsa kuti, “Kodi ufumu wa Mulungu uli ngati chiyani? Kodi Ine ndingawufanizire ndi chiyani?
Yesu naika ati, “Obhukama bhwa Nyamuanga obhususana naki, na enitula okubhususanya na chinuki?
19 Uli ngati mbewu ya mpiru, imene munthu anatenga ndi kudzala mʼmunda mwake. Inakula, nʼkukhala mtengo, ndipo mbalame zamlengalenga zinakhala mʼnthambi zake.”
Obhukama bhunu obhususana na imbibho yo omuharadali eyo omunu agegele nayamba mumugunda gwaye, nimela nilibha eti enene, na jinyonyi ja mulutumba nijumbaka amasuli gajo mumatabhi galyo.
20 Iye anafunsanso kuti, “Kodi ufumu wa Mulungu ndingawufanizire ndi chiyani?
Naika lindi ati, “Nibhususanye naki obhukama bhwa Nyamuanga?
21 Uli ngati yisiti amene mayi anatenga ndi kusakaniza ndi ufa wambiri mpaka anafufumitsa ufawo.”
Obhususana ne echifwimbya echo omugasi agegele nasasha na amakolele gasatu agajinshano nijimala nijitumba.”
22 Ndipo Yesu anayendayenda mʼmizinda ndi mʼmidzi, kumaphunzitsa pamene Iye ankapita ku Yerusalemu.
Namala Yesu nalabha bhuli musi na bhuli chijiji neigishaga ali munjila yokugenda Yerusalemu.
23 Wina anamufunsa Iye kuti, “Ambuye, kodi ndi anthu ochepa okha amene adzapulumutsidwe?” Iye anawawuza kuti,
Omunu umwi nabhusha ati, “Lata Bhugenyi, ni bhanu bhatoto bhanu bhalichunguka?” Kulwejo nabhabhwila ati,
24 “Yesetsani kulowa pa khomo lopapatiza, chifukwa ndikukuwuzani kuti ambiri adzafuna kulowa koma sadzatha kutero.
“Mwikomeshe okwingila mulabhile mumulyango omufunde, kulwokubha abhafu bhalilegeja nawe bhatalingila.
25 Nthawi yomwe mwini nyumba adzayimirira ndi kutseka chitseko, inu mudzayima kunja kugogoda ndi kudandaula kuti, ‘Bwana, tatitsekulirani khomo.’ “Koma Iye adzayankha kuti, ‘Ine sindikukudziwani ndipo sindikudziwanso kumene mwachokera.’
Akefula kanya nyumba nemelegulu negala omulyango, mbe mulimelegulu anja no okukonona kumulyango nimwaika ati, 'Kanyamusi, Kanyamusi, chigulile,' omwene alibhasubhya naika ati, 'nitabhamenya nolwo eyo okusoka.'
26 “Ndipo inu mudzati, tinkadya ndi kumwa ndi inu ndipo munkaphunzitsa mʼmisewu yathu.
Mbe nio mulyaika ati, 'Chaliga nichilya imbele yao kawe nufundishaga mubhyalo bhyeswe.'
27 “Koma Iye adzayankha kuti, ‘Ine sindikukudziwani ndipo sindikudziwanso kumene mwachokera. Chokereni inu nonse ochita zoyipa!’
Nawe omwenene alibhasubhya ati, 'enibhabhwila ati nitakubhamenya amwi neyo omukusoka, musoke kwanye emwe bhanu omukola ebhijabhi!'
28 “Mudzalira ndi kukuta mano mukadzaona Abrahamu, Isake ndi Yakobo ndi aneneri onse ali mu ufumu wa Mulungu koma inuyo mutaponyedwa kunja.
Kulibhao okulila no okuyekenya ameno mulilola Abramu, Isaka, Yakobo na abhalagi bhona mu bhukama bhwa Nyamuanga, nawe emwe mulasilwe anja.
29 Anthu adzachokera kummawa ndi kumadzulo, kumpoto ndi kummwera, kudzakhala pa phwando mu ufumu wa Mulungu.
Abhanu bhalikinga okusoka Ebhutuluka, Ebhugwa, Mubhuanga na Mumalimbe, nibhafung'ama kumeja ye ebhilyo bhya kegolo mu bhukama bhwa Nyamuanga.
30 Ndithudi otsirizira ndiye adzakhale oyambirira, ndipo oyambirira ndiye adzakhale otsirizira.”
Mbe mumenye linu, obhokumalisha bhalibha bhokwamba, na abhokwamba bhalibha bhokumalisha.”
31 Pa nthawi imeneyo Afarisi anabwera kwa Yesu ndipo anati kwa Iye, “Chokani malo ano ndipo pitani kumalo ena aliwonse. Herode akufuna kukuphani.”
Gwejile gwalabhao mwanya mufui, nibhaja Abhafarisayo abhandi nibhamubhwila ati, “Libhata osokanu kulwokubha Herode Kenda okukwita.”
32 Iye anayankha kuti, “Pitani kawuzeni nkhandweyo, Ine ndikutulutsa ziwanda ndi kuchiritsa anthu lero ndi mawa ndipo tsiku lachitatu ndidzakwaniritsa cholinga changa.”
Yesu naika ati, “Mugende mubhwile likara elyo, 'Lola, enibhilimya amasambwa nokuosha abhanu lelo na mutondo, na kulunaku lwa kasatu enikumisha emisango jani.
33 Mʼnjira ina iliyonse, Ine ndiyenera kupitirira ulendo wanga lero, mawa ndi mkuja. Zoona nʼzakuti mneneri sangafere kunja kwa Yerusalemu.
Kumwanya gwonagwona, nikisi kwanye okugendelela lelo, mutondo ne ejweli, kulwokubha jitakwendwa okwita omulagi alikula na Yerusalemu.
34 Iwe Yerusalemu, Yerusalemu! Umapha aneneri ndi kuwagenda miyala anthu amene atumizidwa kwa iwe. Nthawi zambiri ndakhala ndikufuna kusonkhanitsa ana ako pamodzi, monga nkhuku imasonkhanitsira anapiye pansi pa mapiko ake, koma iwe sunafune!
Yerusalemu, Yerusalemu, awe unu wetile abhalagi nokubhabhuma na amabhui bhanu bhatumilwe kwimwe. Kwiya ng'endo elinga ninendaga okusumbya abhana bhao amwi lwakutyo ing'oko eisumbya ebhyanakoko bhyayo mumbabha jayo, nawe mwaliga mutakwenda.
35 Taona, nyumba yako yasanduka bwinja. Ine ndikukuwuza kuti, sudzandionanso mpaka pamene udzati, “Wodala amene akubwera mʼdzina la Ambuye!”
Lola inyumba yao yasigwa yenyele. Mbe enikubhwila, mutachandola lindi okukinga olwo mulyaika ati, 'Ana amabhando oyo ejile kwi Sina lyo Omukama.”'